Mwera: Bible for Acts

Formatted for Translators

©2022 Wycliffe Associates
Released under a Creative Commons Attribution-ShareAlike 4.0 International License.
Bible Text: The English Unlocked Literal Bible (ULB)
©2017 Wycliffe Associates
Available at https://bibleineverylanguage.org/translations
The English Unlocked Literal Bible is based on the unfoldingWord® Literal Text, CC BY-SA 4.0. The original work of the unfoldingWord® Literal Text is available at https://unfoldingword.bible/ult/.
The ULB is licensed under the Creative Commons Attribution-ShareAlike 4.0 International License.
Notes: English ULB Translation Notes
©2017 Wycliffe Associates
Available at https://bibleineverylanguage.org/translations
The English ULB Translation Notes is based on the unfoldingWord translationNotes, under CC BY-SA 4.0. The original unfoldingWord work is available at https://unfoldingword.bible/utn.
The ULB Notes is licensed under the Creative Commons Attribution-ShareAlike 4.0 International License.
To view a copy of the CC BY-SA 4.0 license visit http://creativecommons.org/licenses/by-sa/4.0/
Below is a human-readable summary of (and not a substitute for) the license.
You are free to:
The licensor cannot revoke these freedoms as long as you follow the license terms.
Under the following conditions:
Notices:
You do not have to comply with the license for elements of the material in the public domain or where your use is permitted by an applicable exception or limitation.
No warranties are given. The license may not give you all of the permissions necessary for your intended use. For example, other rights such as publicity, privacy, or moral rights may limit how you use the material.

Acts

Chapter 1

1 Chitabu chija choyamba nidachilemba Theofilo katika mau yonje adaloyayamba nnunu kuchita nikuyaluza. 2 Hata siku lija wadatotengedwa kumwamba pajawalipo wadatokwisha kuwagiza kwa mtima mtakatifu waya mitume wajadawachagua. 3 Waja wadatothibitisha nafsi yaiye kwa dalili zambili baada yateswa kwake ya kwamba yu wamoyo akiwatumikila muda wa siku arobaijni na kkamba mau yajayausu ufalume wa Mulungu. 4 Hata pajawadali wadatopezana nao adatowaagiza siwadachoka Payerusalemu bali walindilile ahadi ya baba ambapo mdatovela habari zake kwaine. 5 Ya kwamba Yohana wadatobatiza kwa maji bali anyiinu simbatizwe katika Mzimu Woyela baada ya siku zing'ono.'' 6 Basi pajawatopezana wadamfunja wamatokamba, je bwana nyakati hizi ndipo siwabwezele Israeli ufalume? 7 Adatowakambila, si njito yanu kujiwa nyakati wala majira baba yajawadayaika katika mamlaka yaiye mwene. 8 Lakini simlandile mbavu juu yanu Mzimu Woyela naanyiinu simuwe mashahidi waine katika Yerusalemu na katika Uyahudi wonje na Samaria na hata potela pa nchi.'' 9 Ambuye Yesu yapoadatha kukamba yaya, Adali apenya kumwamba, iye wadanyakulidwa kumwamba. Ndi mitambo idamvinikila kuthi asamuona kwa maso yao. 10 Nyengo amapenya kumwamba bwino bwino wamamapita mwazizi, wanthu awili adaima mkatikati mwa anyaio avala nchalu zoela. 11 Adakamba, "anyaimwa wanthu Akugalilaya , ndande chiyani mwaima yapa uku ndi mpenya kumwamba?" Yawa Ambuye Yesu apululukila kumwamba siwabwele kwa mtundu umweuja mudamwonela yapo wamapita kumwamba. 12 Ndeyapo adabwela ku Yerusalemu kuchokela kupili la mizeituni, lili patupi ndi Yerusalemu endedwe la siku lopempha. 13 Yapo adafika adapita kumwamba uko amakala nao nde Petro, Yohana, Yakobo, Andrea, Filipo, Tomaso, Batholomayo, Mathayo, Yakobo mwana wa Alfayo, Simon Zelote ndi Yuda mwana wa Yakobo. 14 Onche adagwilana ngati munthu mmojhi, pakuti mbila adaendekela ndi mapemphelo. Pamoji ndi anyiayo adalipo wachikhazi, MAriamu amake wa Ambuye Yesu ndi achakulu wake. 15 Pa nyengo zija Petro wadaima pa katikati panga, ngati wanthu 120, wadakamba. 16 Achabale, idali uune, usauna malembo yakwanile, yapo kale mzimu oyela udakamba kupitila mlomo wa Daudi pakati pa Yuda, iye wadaakambila anyiao ada mkana Yesu. 17 Pakuti iye wadali mmojhi wa ife ndi wadalandila ungo lake la pindu mkati mwa chitandizo.'' 18 (Chipano munthu uyu wadakwezedwa pamale kwa pachijha wadalandila pa uomboli wake ndeyapho wadagwa uku wachogoza muthu thupi lidasweka ndi matumbo yake yonche yadali pooneka ndikumwazika. 19 Onche amakhala ku Yerusalemu adavela, kwaicho malo yameneyo adapata kwa mkambo "Akeldama" kuti munda wa magazi.'') 20 mchikalakala cha zaburi mwalembedwa linda malo yake yakale masame ndi pasalolezedwa muthu kukalapo pajna ndiloleza muthu mwina watenge malo yake ya udindo.' 21 Iyinde yofunika kwaicho mmoji wawachimuna wadachoghozama ndi ife nyengo Ambuye Yesu yapo adachoka ndi kulolwa mkati mwathu 22 Chiyambili kutilidwa maji kwa Yohana mbakana siku lija wadatengedwa juu ifunika wakhale mboni wa kuhyuka pamoji kati katindi ife 23 Wadaika pachogholo wachimuna awili Yusufu watanidwa Banarba wamatanidwa yusto ndi matia. 24 Anyaio adapempha ndi kunena imwa Ambuye mujhiwa mitima ya wanthu wonche kwaichi ikani pa danga yuti kati ya awili yawa mwamsankha. 25 Kutinga malo ya chitandizo ndi utumiki nyengo Yuda wadachita volakwa ndi kupita pamalo pake. 26 Adachita chisanko kwa ndande zao ndi chisanko chidamgwela matia wadawelengedwa pamojhi ndi anyaiwo atumiki kumi ndi mmojhi.

Chapter 2

1 Yapo yadafika siku la Pentekosita, wonche adali malo amoji. 2 Mwaziziizi kudamuka mau ochokela kumisamba ngati mphep yayikulu nijaza nyumba yonche makhalama wanthu. 3 Pamenepo kwayio ngati malilime a moto ziganizidwa zidali pamwamba pawo, aliyembe wake wake. 4 Ino adajazidwa ndi mzimu woyela ndi adayamba kukamba mikambo yosayana soyana ngati mmene mzimu adawakambisa. 5 Nchipano padalepo Ayahudi amene amakhala Muyerusalemu , apempha Mulungu ochokela kila jhiko pansi pa thambo. 6 Phokoso yili yapo lidaveka, anthu ambili kolabwela pamoji adali ndi kukayika, chifuko munthu aliyenche adawavela akukamba pa mkambo wakewake. 7 Anadabwa ndi kuzizwa, adanena kuti onche yawa sati Agalilea kodi? 8 Chifuko chiyani ife tiwamvela akukamba aliyenche chimkambo cha kwawo. 9 Waparthi ndi Amedi ndi iwo okhala Kumasipotamia Uyahudi ndi Kukapadokia ndi Ponto ndi Asia. 10 Ndi Frigia pafulia ndi ku Misili, ndi mbali ya Libia ndi Krene ndi alendo achokela ku Roma. 11 Wayahudi ndi na Akrete ndi Walabu yao tikuvela akukamba mumkambo yathu za nchite za phamvu za Mulungu.'' 12 Onse adazizwa ndi kudabwa adakambilana wina ndi mzake, "kodi chimenechi ndi chiyani?" 13 Kona ena amasaka ndikuti "yawa akhuta vunyo wa lero." 14 Koma Petro adakamba pamoj ndi khumi ndi mmjhi, adakkoza mau, adakamba Ayida onu ndi ontche okhala, muno mu Yerusalemu. Velani ndipo muvechetche mau yanga. 15 Wanthu yawa salizele ngati mganizia imwe pakuti nthawi ya wana saa tatu umawa. 16 Koma zidayenela kuchitidwa zokambdwa ndi Yoelmmenel. 17 Pazafika masiku othera, Mulungu azakamba ndizathira mzimu wanga kwa wanthu ontche. Wana wanu wamuna ndi akazi azanenela anyamata aezaona vinthu mmasophenya ndi abambo azezalota malota. 18 Ngakhale pa anchita wanga ndi anchito wa atate wang. Ozakhala masiku amenewo ndizathela mzimu wanga ndi iwo azalalika. 19 Ndi za oncha vodibwicha kumwamba ndi vizindikilo pajiko, mwazi moto ndi ulchi toro. 20 Juwa lizakhala madima ndi mzozi uzakhala mdima, lisadafike siku la likulu la Ambuye. 21 Lizakhala kuti aliyenche akayatana pa jino la Ambuye azapulumuka.' 22 Wanthu a Israeli yomwe, velani mau yaya, Yesu Mnazaleti adali munthu uyu Mulungu adamutuma kwa yomwe. Mulungu adakutchumikizatani vimenevo ndi vaphamvu, vodabwitcha ndi vizindikilo vivo adachita kupitila mwa yiyeyo pakati panu umo mujiwila. 23 Kwachifukwa cha maganizo yadalipo kuyambila ndi njelu za Mulungu, adacholchodwa ndi yimwe kwa wnthu owononga, adamphachika ndi kumupha. 24 Yomwe Mulungu adamukweza kumuchotcha kuzozoawa za nyifa yake. Chifuko sikundi kutheka kuti iye agwichoe ndi awanthu oipa. 25 Mmwemo Daudi adakamba za iye nidamuona mbuye nthawi zonse pamaso penga, iye ali kuzonje langa lamanja kuti ndi sinthidwe. 26 Chifukwa mtima wanga adili ndi chisangalalo ndi lilime langa udakondwela, ndiso thupi langa langa lizalama ndi chiyembekezo. 27 Siuzaisiya moyo wanga ku hade, ndi suzolola semuzalole woyela wanu kuti aone choola. 28 Mudandiziwisa ine, njala za moyo, uzazichita nizzichwe ndo chisangalalo pamaso panu.' 29 Amuna yimwe, ndikhoza kukamba choonadi ndi phamvu. chifuko atate wanthu DAvidi, iye adafa adayikidwa m'manda, ndi manda ake alipo mpakana pano pakati pathu. 30 Mmene anali mneneli, ndi adaziwa kuti Mulungu adatha kulumbila, kulumbila kwake kuti azaika mmojhi pakati pa mibadwa wake pampando wachifumu. 31 Pamene adaona zimenezi mwambanga, ndi adakamba pamwamba kuuka kwa Kristo, ndisadasiyichwe kwa akufa ndi thupi lake silidaole.' 32 Iye Yesu Mulungu adamuukisa, amene ife taonche ndi mboni. 33 Potheza adakwezechwa ndi janja la kwene la Mulungu, nalandila chipangano cha mzimu oyela, kuchokela kwa atate, iye athela pangano imene yemnoe mudaiona ndi kuvela. 34 Pakuti Davidi sadakwele kumwamba ayi, kama adanena, Ambuye akuti kwa Mbuye wana, khala ku jenje langa la kwene. 35 Mbakana pamene ndizaika adani ako chopondapo mapazi yako. 36 Mmwemo mnyumba yontcho ya Israeli yozewe kuti uzene Mulungu wanchita iye kukhala Mbuye ndi Kristo. Iye Yesu amene mdanpachika.'' 37 Sopano pamene adamva zimenezi, adalasxidwa mmutima yawo, adamkambila Petro ndi atumwi ena waje abale tichite chiyani? 38 Petro adali "lapani ni kubatizidwa aliyenche mjina la Yesu Kristo kupita kukulekeledwa kwa zambi zanu, ndi kupheza mphaso ya Mzimu Woyela. 39 Pakuti chipangano alili kwa imwe ndi achiwana wanu ndi kwa ontche ikhala kutari ndi kwawo, ndi ontche Ambuye Mulungu azatana." 40 Kwa mau amenewa adachita umboni nawadandaulila iwe akamba jipulumusini kum'bacho okholakhola. 41 Pamenepo iwo adalandila mau yake adabatizidwa ndipo adaonjezedwa wanthu ngati elfu tatu. 42 Ndipo adapitilila kukhala mchipunziso cha alumwi ndi cheyanjano chimoji kumneyo mkate ndi kupemphela. 43 Koma panabwela mantha pawanthu ontche ndipo vodabwitche ndi vizindiklo vadachidwando wanafunzi. 44 Ontche adakhulupilila adali pamoji ndi kukhala ndo vimthu vawo pamoji. 45 Ni adagulicha vanthu aneli navo ndi monela yawo na gawila au'mphawi, mmena adafunila. 46 Mmenemo siku ndi adapitilila ndi maganizo amoji mu hekalu, ndi adatyola mkate ku nyumba zawo ndo adalandila chakudya ndi msangala ndi mtima wona. 47 Anamkweza Mulungu ndi kukhala ndi kubali ndi wanthu ontche , Ambuye adaonjezela wanthu sikundi siku amene adapulumuchidwa.

Chapter 3

1 Chapano Petro ndi Yohana adali ndiapita paui malopa mapemphelo nthawi yopemphela saa tisa. 2 Munthu wakuti wosayenda chibadwile. Wadalindi wabalidwa masiku yonche ndi wadali ndi wagonekedwa pakati pachicheko cha malo yopemphela ya mene yatanidwa mzuri dala kuti wakoze kupempha sadaka kuchokala kwawanthu amapita kunyumba ya mapemphelo. 3 Yapo wadaona Petro ndi Yohana awandikila kulowa mnyumba ya mapemphelo wadapempha sadaka. 4 Petro wadampenyechecha kupunda pamoji ndi Yohana wadamkambila, "tipenye ife." 5 Munthu wosayenda wada apenya ndiwa kurupalila kulandila chinthu cha kuti kuchokela kwa anyaiwo. 6 Nampho Petro wadakamba, "ndalama ndi chuma ine ndilije nampho chiwene ndilinacho sindikupweche iwe pakati pa jina la Yesu Kristo wa KUnazareti yenda." 7 Petro wadamtenga pa janja lakela kwene ndi kumkweza kumwamba ntawi kamoji miendo yake ndi vipombono vake va vifupa vake vidapeza mphavu. 8 Ndi wammpa kumwamba, munthu osayenda waalowa mapempelela pamoji ndi Petro ndi Yohana ndi walumpa ndi kumuyamika Mulungu. 9 Wanthu onche adamuone ndiwayenda ndikumkwezeka Mulungu. 10 Adajiwa kuti wadali muntu yuja siwamayende wamango kala ndiwapempha sadaka mchicheko cha bwino cha malo ya mapemphelo adajalidwa ndi kuzizwa ndi osazindikil chimene chachitika chifukwa chimene chachokela kwaiye. 11 Mtundu umo wadali wa agwililila Petro ndi Yohana wanthu wonche kwa umoi wao adatamangila malo yokomenila wa yatanidwa, wa Yerusalemu ndi azizwa kupunda. 12 Petro yapo wadaona ichi iye wadaayankha wanthu, anyiimwe wanthu wa Muisraeli chifukwa chiyani muzizwa? Chifukwa chiyani masoyani yapempha viwi kwa ife ngati kuti ife nde tamchita uyu wayende kwa mphavu zatu tawefe kapena maelekedwe yatu?'' 13 Mulungu wa Ibrahimu ndi wa Isaka ndi wa Yakobo, Mulungu waache atate watu amolemekeza mtumiki wake Yesu uyo ndi mmene anyaimwe mnampacho ndi kumkana pamaso pa Pilato. Ingakale iye wadalamula wasiidwe. 14 Muda mkano munthu oyela ndi wali ndi ulamulilo pambuyo pake mdafuna munthu wakupa vasiilidwe. 15 Anyaimwe mdamupa furu wa mtendele mmene Mulngu wadamzusha kuchokela kwa wanthu adafa ife ndi amboni aili. 16 Chapano kwa chikhulupi pakati pa jina lake munthu uyu umuona ndikujiwa, wadachitidwa kukala ndimphavu chikhulupi chimene chipitila kwa Yesu yampacha iye mtendele wabwino pachogolo panu anyaimwe mwaonche. 17 Chapano abale ndijiwa kuti mdachita pakati pausajiwa mwemo umo adachitila achogoleli wanu. 18 Nampho vichito vine Mulungu wadakukambilani mwamsanga mwamkamwa mwa olota onche kuti uyu Kristo siwavutike chapano ya kwanila. 19 Kwaicho lapani ndi mng'anamke dala kuti machimo yanu yakoze kuchochedwa yonche dala kuti zibwele nyengo zo sangalala kuchokela kukalapo kwa atate. 20 Ndikuti wakoze kumtuma Kristo mmewa saukulidwa kwa chifukwa,Chanu. 21 Iyeyo ndimmeneyo chichimichimi jhiko limlandile mpaka nthawi ya kubwezedwela vinthu vonche vimene Mulungu wadavikambila engo za kalekale kwa mkamwa mwa olota oyela. 22 Chazene Musa wadakamba Mulungu siwmkweze olota ngati ine kuchokela mwacha abale wanu, simumvenchele chilichonche chimene siwakukambileni anyaimwe. 23 Siichokele kuti munthu waliyenhe siwavecha kwa olota mmene siwasowechedwe wochoke pakati pawanthu.' 24 Yetu, olota oche chichokele Samweli ndi anyiwaa adachatila pambuyo pake odakamba ndi adalalikila nthawi izi. 25 Anyaimwe wana wa olota ndi pangizo limene Mulungu wadalichita ndi anya Ambuye ngati ume wadakambila kwa Abraham, "pakati mbeu yako ndi fuko lonche mjiko sizing'anamuka. 26 Pambuyo pa Mulungu kumkweza mtumiki wake wadamtuma kwa anyaimwe poyamba dalakuti mpachidwe mwawi anyaimwe kwa kunganamuka pakati pa voipa vanu."

Chapter 4

1 Nyengo Petro ndi Yohana yapoadali mkucheza ndi wandhu, anchembhe ndi olonda wa Hekalu ndi Masadukayo adawaendela. 2 Adali aipila kupunda kwa ndande Petro ndi Yohana adali mkuwayaluza wandhu kukuza. Yesu ndi kulalika pamwamba pa kuhyuka kwaiye kuchokela kwa akufa. 3 Adwagwila ndi kuwaika mgerezampakane umawa ochatila chifuko mokwanila idali mjhulo. 4 Nampho wandhu ambili yawodali kuvecha utenga adakulupilila ndi uyinji wa wachimuna yawo adala atokukulupalila, adaganizidwa adali elfu zisano. 5 Ingakale yapo idafika umawa sikuidachafila, kuti wakuluwakulu wawo, midala ndi ohemba, kwa pamojhi adakamana kuiyerusalemu. 6 anasi wamkulu wa nchembe wa dalipo ndi kayafa, udi yoana ndi iskanda, ndi wohehe yawadali ndi achebele wa wamkulu wa nchembe . 7 yapoadali awaika petro ndi yohana pakefikati pauo, adafujhe kwa kukoza kutikapena kwa jhina liti mwachite hili?'' 8 Ndipo Petro yapowadahala i wajhala mzimu oyela adkambila, "anyiimwe wakuluwakulu wa wandhu, ndi midala. 9 Ngati ife siku yadelo tichimikizidwa kukuza ichitidwe la bwino lidachitidwa kwa mundhu uyu odwala kwa ntundu uti mundhu uyu wadachitidwa umoyo? 10 Ebu lijhulikane limenelo kwanu ndi kwa wandhu wonche wa Israeli kuti kwa jhina la Yesu Kristo wa Nazareti, uyo mdamtalamicha uyo Mulungu wadamhyucha kuchokela kchoka kwa akufa, ndi kwa njila yake kuti mundhu uyu waima pano pachogolo panu ndiwakala wa tanzi. 11 Yesu Kristo ndi mwala uwo anyiiwe omanga mdalipepula nampho ilo lachitidwa kukala mwala wa ukulu wa mphepete. 12 Palibe chipulumuchi pa wandhu mwena waliyenche. Kwa mate palibe jhina lena pajhi pa jhiko apachidwa wandhu, iho kwa limenelo tikoza kupulumuchidwa." 13 Chipano yapoadaona kulimbilika kwa Petro ndi Yohana adajhiwa kuti adali ndi wandhu achimwechi opande njelu, adazizwa adajhiwa kti Petro ndi Yohana adal pamojhi ndi Yesu. 14 Kwa ndande adamuona yujha mundhu wadalamichidwa waima pamojhi nawo si adali ndi chindhu cha kunena kupitilila ili. 15 Nampho yapoadali ato kuwalamula atumi achoke pachogolo pa agulu ndi bwalo, adanena anyiiwo kwa anyiiwo. 16 Adanena, sitiachitebwanji wandhu yawa? Ndi zene kuti chidabwecho chodabwicha chachitika kupitila anyiiwo ajhulikana ndi kila mmojhi wakala Kuyerusalemu, sitikoza kulikana limenelo. 17 Nampho, kuti chitidwe ili lisidenela mmojhi mwa wandhu ebu sianyindile asadanenancho kwa wandhu waliyenche kwa jhino ili. 18 Adatanidwa Petro ndi Yohana mkati ndi kuwalamulila asanena wala kuyaluza kwa jhina la Yesu. 19 Nampho Petro ndi Yohana wadayankha ndi kwakambila, "ngati ngati ndi uzene pamaso pa Mulungu kukovomelezani anyiimwe kupunda Mulungu, lamulani mwachiawene. 20 Chifuko ife sitikoza kusiya kuyanena yochitika yayo tayaona ndi kuyavela." 21 Pambuyo pa kuwanena kupunda Petro ndi Yohana adasiya ajhipita. Siadakoze kupeza ndande yaliyonche ya kuwalamula kwa ndande wandhu wonche adali kunikoza Mulungu kwa chijha chidali kuchijidwa. 22 Mundhu uyowadali kulandila chodabwicha cha kuamichidwa wadapezekova kukala ndi msigu opitilila ndi vyaka arobaini. 23 Pambuyo pa kwasiya osililidwa, Petro ndi Yohana adajha kwa wandhu wawo ndi kuwaajhinicha yonche yayo wakuluakulu anchembe ndi midela adali kuwakambila. 24 Yapoadavela, adakuza mau yawo kwa pamojhi kwa Mulungu ndi kunena, "Ambuye imwe mwa panga kumwamba ndi jhiko ndi nyanja ndi kila chinthu mkati mwake. 25 Iwe mmeneyo kwa mzimu oyela kwa pakawa, pa atate watu Daudi mtumiki wa iwe, udanena, ""kwa ndande chiyani wandhu wa ajhiko achita mavulukutyundi wandhu aganizila vichito vosafunike? 26 Mafumu ajhiko ali pamojhi ndi olamula ali pamojhi pa limojhi ndi wandhu wa mayiko wandhu wa Kuisrali adakomana kwa pamojhi kupitilila atate ndi kupitilila mashili wa iye." 27 Ndi chichimichimi wonche Herode ndi Pontio Pilato, pamojhi ndi wandhu wa mayiko ndi wandhu wa Israeli, adapezekekana pamojhi pa mujhi umene kupitilila mtumiki wa iwe oyela Yesu, uyoudamtyeka mafuta. 28 Adapezekana kwa pamojhi kuchita yonche yayo jhanja lano ndi chikondi chikondi chako chidalamulira kuyambila mmayambo kabla siyadachokele. 29 Chipano atate, yapenyeni yoofecha yawo, ndi ukawapache watumi waiwe kulinenamau lako posaope wonche kuti. 30 Yapoutambaseila jhanja lako kulamicha, chizindikilo ndi vodabwicha vikoze kuchokela kupitila jhina la mtumi wako oyela Yesu. 31 Yapo adamaliza kuphembela, malo yayo adasoghana kwa palimojhi lidatingizidwa ndi wonche adajhazidwa ndi mzimu oyela ndi kunena mau la Mulungu popande kuopa. 32 Gulu lalikulu ya anyiwajha adakulupalila adali ndi mtima umojhi ndi mzimu umojhi ndi palibe ata mmojhi wanyiiwo wadanenakuti chalichonche ichochilimmonja murake chidali cha iye mwene wake. Pambuyo pake adali ndi vindhu vonche paumojhi. 33 Kwa mphavu yaikulu atumi adali kulalikila umboni wano kukua kuyhuka kwa atate watu Yesu, ndi kulandila kwa kukulu kudali pamwamba pao wonche. 34 Padali popande ndi mundhu waliyeche mwanyiiwo wadatedwa ndi vopata, kwa ndande wandhu wonche yao adali ndi chiwembu kumbu cha maliwalakapena nyumba, adavigulicha ndi kupeleka ndalama ya vindhu ivo adavigulicha. 35 Ndi kuviika panchi pa myendo ya otumidwa. Ndi kaganidwe kadachitidwa kwa oklupalila, kuchana ndi kila mmojhi ivo wa mavifuna. 36 Yusufu Mlawi, mundhu kchokela Kukiproadapachidwa jhina la Barnabasi ndi atumiki (imeneyo idatafisilidwa, ndi mwana wa faraja). 37 Yapowadali ndi munda adaligulicha ndi kupeleka ndalama, kuziika panchi pa myendo ya otumidwa.

Chapter 5

1 Kwa icho munthu mmojhi wamatanidwa Anania ndi Safira mkazake adagulicha munda wao. 2 Ndi kubisa ndarama ya kmoi (mkazake wamajiwa) wadapeleka idakale ndi kuiika mmyendo mwa otumidwa. 3 Nampho Petro wadakamba, "Anania ndande chiyani satana wauchita mtima wakokukamba unami kwa mzimu oyela ndi kubisa chuma cha kumojhi cha munda." 4 Nyengo ukali osaguliche, idali osati chuma chako ndi nyapo wagulicha chidali osati panchi pa lamulo lako? Ikala bwanji uganize chinthu ichi mumtima mwako? Siudaanyenge wanthu na wamnyenga Mlungu? 5 Povela mau yaya, Anania wadagwa panchi ndi kufa mantha yaajela wanthu onche adavela nkhani iyi. 6 Anyamata adaja pachogolo ndi kumveka senda ndi kumpeleka kubwalo ndi kumzika. 7 Pambuyo pa masaa yatatu, mkazake wadalowa mkati siwajiwa icho chachokela. 8 Petro wadamkambila, nikambile ngati mwagulicha munda kwa mtengo huu, wadakamba "yetu ntengo umweo." 9 Petro wadamkambila, ikala bwanji mavana kumuyesa mzimu wa Ambuye? Penya myendo yao umzika mmunako ili pakomo, sakubale ndi kukupeleka kubwalo. 10 Mwachizulumikila wadagwa pamyendo pa Petro ndi kumwalila, anyamata waja adaja mnyumba ndi kumpeza wafa, adam'bala ndi kumpelea ndi kubwalo ndi kumzika pafupi ndi mmunake. 11 Mantha yambili yyadaja kanisalonche ndi kwa wanthu onche adavela nkhani iyi. 12 Vodabwicha vambili vidachokela mkati mwa wanthu kupitila manja ya otumdwa, adali pamoji mu ukumbi wa Suleman. 13 Nampho palibe munthu mwina wa payoka walimbikila kuchatana nao, ingakale chimwecho adapachidwa ulemu wa pamwamba ndi wanthu. 14 Okulupilila ambili adachuluka kwa Ambuye wachimuna ndi wachikazi. 15 Kuti adatenga odwala ndi kuaika mmachikandi mmipando kuti Petro yapo siwajipita chitu nchi chake chikale pamwamba pao. 16 Pamenepo wanthu ambili adaja kuchokela miji yazungulila Yerusalemu, adapeleka odwala ndi yao ali ndi mizimu yoipa, onche adachilisidwa. 17 Nampho wamkulu wanchembe wadaima ndi wanthu wadali nao pamojhi (Masadukayo) ;adajalanche. 18 Adatambasula, anja ya kuagwila otumidwa ndi kuaika mkati mwa ndande. 19 Ndi nyengo ya usiku angelo wa Ambuye wadachakula vicheko va ndande ndi kuachogoza kubwalo ndi kukamba. 20 Pitani mkaima mu hekalu ndi kuakambila warithu mau yonche ya umoyo uu. 21 Yapo adavela chimwechi adalowa mu muhekalu mjengo ya mmalenga kucha ndi kuyaluza nampho wamkulu wa nchambe wadaja ndi onche wagalinao ndikutanicha baraza loche pamoji ndi okota oncha wa lsraeli ndi kuatumakundanda kukaatenda otumidwa. 22 Nampho atumiki yao adapita saadaapeze kundende adabwala ndi kupeleka mayankho, 23 "Tapeza ndande yamangidwa bwino, ndi openyelela aima pakomo, nampho yapo tidachakula sitidaone munthu mkati." 24 Chapano, nyengo wamkulu wa asrikali ahekalu ndi waakuluakulu anchembe, yapo adavela mau yaya adalowedwa ndi mantha saadajiwe icho chaapeza. 25 Munthu mmoji wadaja ndi kuakambila wanthu waja muda aika mndende aima muhekalu atoyaluza.'' 26 Kwa icho wamkulu wa asrikali wadapita pamoja ndi atumiki adajanao nampho saada tenge kwa mphavu ndande amaaopa wanthu, adakabula myala. 27 Adaapeleka ndi kuaimika pa baraza ndi kuakambila. 28 Tidakukanizani kuyaluza kwa jina la munthu uyu nampho mkali, mwaijaliza Yerusalem mayaluzo yanu ndi kukumbila kutiikila pamwamba patu mwazi wa muthu uyu.'' 29 Nampho Petro ndi otumidwa adayankha tifunika kumlemekeza Mulungu opande wanthu. 30 Mlungu wa achiatate watu wadamzyucha yesu mmene nadampa kwa kumuika pamtande. 31 Mlungu adamkuzika ndi kumchite wakalejanjala kwene la Mlungu ndi kumchite wamkulu ndi Mpulumusi ndi okuluhula machimo. 32 Ife ndi mboni wa vinthu ivi ndi Mzimu Oyera mmene Mlungu wa mchocha kwa yao amlekeza.'' 33 Apungua baraza yupo adavela chimwechi adakwiya ndi kufuna kuapa otumidwa. 34 Nampho Farisayo mmoja watanidwa gamalichi mpuzisi wa matauko olemekezeka ndi wanthu onche wadaima ndi kulumula otumidwa ochochedwe kubwalo kwa nthawi yaifupi. 35 Wadakambila wachimuna a Israel jipenyeleleni ndi chimene mfuna kuachita wanthuyawa. 36 Ndande kale lopita theuda wadaima ndikujichita munthu wamkulu wanthu mianne adali kumbuyo kwake wadapedwa ndi yao amani chata onche adasowa . 37 Pambuyo pake yuda mgalile mjengo yowlenga wanthu wadaaguza wanthu ambili ndi pambuyo nae wadapedwa ndi gulu loche lidasowa. 38 Chapano nikukambilani kalani kumphepete ndi wanthu yawa mwaiye achinawene ndande ngati nchito ya wanthu sutaidwe. 39 Nampho ngati nchito uji ndi ya Mlungu simkoza kuitimika mkoza kujipeza mpikisana ndi miungu kwa icho adavomelezana ndi mau yake. 40 Kwa icho adaatana otumidwa mkati ndik atyapa ndi kualamula, asadanenancho mu jina la Yesu ndi kuasiya ajipita. 41 Adachoka ndi chimwemwe chifukwa awelengedwa aenela kuvutika ndi osalemekezedwa ndande ya jina la Yesu. 42 Kwa icho, kila siku, mkati mwa hekalu ndi kuchokela nyumba mbaka nyumba adaendekela kuyaluza ndi kulalika kuti Yesu ndi Mpulumusi.

Chapter 6

1 Chipano pakati pa siku zino nyengo idadi ya opuzila idaongezeka malundu wa Ayahudi wa Kiyunani udayamba pakati Waebrania kwa chifuko ofendwa ndi wachimuna anyaio amayowalika pakati po gawana chakudya kila sku. 2 Atumiki kumi ndi awili adaudatana msonkhano onche wa opuzila ndi kukamba osati uzene kwatu kulisiya mau la Mulungu ndi kuthandiza pameza. 3 Kwa chimwecho bale sankhulani waachimuna saba kuchokela pakati panu wanthu abwino anyiyao ajhalidwa mzimu ndi ulemu yao tikhoza kwapacha matandizo uu. 4 Ndi ife tiendekelela nyengo kupempha pakati pa mthandizo wa mau.'' 5 Hotuba yao idaukwadilicha msonkhano onche chimwecho adamsankha Stefano wadajalwa ndi chikhulupi ndi mzimu oyela ndi Filipo Prokoro Nikanori Timoni Parmena ndi nikalao kupulumika kuchokela ku antiokia. 6 Akristo wadapeleka wanthu yawa pachogolo pa atumiki yao adapempha ndi pambuyo wadaakila manja yao. 7 Chimweko mau la mulungu lindaenela ndi idadi ya opuzila idapunda kukuongezeka kumeneko Kuyesrusalemu ndi idadi yaikulu ya makuhani adachivomela. 8 Ndi Stefano wadajhalidwa ndi mwawi ndi mphavu wamachita vozizwicha ndi langizo lalikulu pakati pa wanthu. 9 Nampho pamenepo adakuela wanthu akumojli ochata asinagogi ilo litanidwa sinagogi la Mahuru ndi la Akirene ndi la Waeskanderia ndi wina adali naafunchana ndi Stefano. 10 Nampho saadakhoze kushindaa ndi ulemu ndi mzimu uwo Stefano wamatumikila pakati pokamba. 11 Pothela pake wadaanyenga wanthu wina kwa chisisi kukamba tavela Stefano niwakamba mauya mwano pakati pa musa ndi pakati pa Mulungu.'' 12 Wadaalamula wanthu azee ndi olemba olemba ndi kumpitila Stefano adamgwila ndi kumpeleka pachogolo pa bwalo. 13 Wadaapeleka amboni aunami yavadakamba munthu uyu siwasia kukamba mau yaipa pakati pa malo yaya yoela ndi thauko. 14 Kwani tamvela niwakamba kti uyu Yesu wa kunazareti siwapawanage pamalo pano ndi kuzing'anamula destuli izozakabizidwa ndi musa. 15 Kila mmojhi uyo wadali pakatika bwalo wadayapoleka maso yake kumpemya stefano nao adiaina mphumi yake idali ngati mpumi ya angelo.

Chapter 7

1 Kuhani wamkulu wadakamba, "vinthu ivi ni va kweli?" 2 Stefano wakamba, "abale ndi anya Ambuye wanga, niveleni ine: Mulungu wa chimwemwe wadamchokela Mbuye watu Abrahamu dyawi yapowali Mesopotamia, kabla siwalame kuharani. 3 Adamkambila chokapo, katika jiko lako ndi jama zako ndiupite jiko ilosinikulangize.' 4 Potela wadachoka jiko la wakala Kuharani, kuchokela pamenepo, baada ya acha Ambuye wake kumwalila, Mulungu adampeleka kujiko ilo, iloakala chipano. 5 Siwadampache chalichonche ngati ulithi wake, sipadakale ndi sehemu hata yakuika myendo. Nampho Abrahamu adamuahidi ata kabla siwadapate mwana kuti siwapachidwe jhiko ngati miiki yake ndi ubazi wake. 6 Mulungu wadanena nae chimwe, yakuti aubazi wake adakakala katika jiko ya ulendo, ndi kuti wenyeji wakuno siachite kukala, atumwa wao ndi kwachita voipa kwa nthawi ya vyaka mia nne. 7 Ndi Mulungu wadakamba, silihukumu taifa ambalo silachite mateka, ndi pambuyo pamenepo siachoke ndi kunigwadila katika sehemu ii. 8 Ndi adampacha Abrahamu agano la tohara, chimwecho Abraham wadali baba wa Isaka adamtaili sikuya nane. Isaka wadali baba wa Yakobo, ndi Yakobo wadali baba wa mababa zanthu kumi ndi awili. 9 Mababu zatu adamwonela nchanje Yusufu adamgulicha katika jiko la Kumisri, ndi Mulungu wadali pamoji nae. 10 Ndi adamlamicha katika mazunjo yake, ndi kumpacha fadhili ndi ulemu pachogolo pa Farao mflume wa Kumisri. Farao adamchita wakale otawala juu ya Misri ndi juu ya nyumba yake yonche. 11 Basi kudali udi ujalu udi mazunjo ya yambili katika jiko la Misri ndi Kanaani ndi mababa zatu siadate chakudya. 12 Nampho Yakobo yapowadavela kuli vakudya kuori Misri adatuma mababa zatu kwamava yoyamba. 13 Katika safali yakawili Yusufu wadajilandiza kwa mabale zake familia ya Yusufu idajulikana kwa Farao. 14 Yusufu wadauma ambale wake kupita kumkambila yakobo babawao wajekumisri pamoji ndi jamaa zake jumla ya wantu onche nisabiini na tano. 15 Chimwecho Yakobo wadachika Kumisri potela wa dafa iye pamoji ndi baba watu. 16 Adatengedwa hata Shekemu adazikidwa katika kaburi ambalo Abrahamu wadaligula kwa vipande va ndalama kuchokela kwa wana wa Harani kumene Kushekemu. 17 Nyengo ya ija ahadi ambapo Mulungu wadamwaidi Abrahamu yapowadasendelela, wanthu adali aongezeka kumene Kumisri. 18 Nyengo imeneyo wadaima mfalume mwina pamwamba pa Misri, mfalume uyosiwajiwa kuhusu Yusufu. 19 Mmene mflume mwina wadanyenga wanthu watu ndi kwachita voipa baba, ndi kwataya wana wao akanda ili siamoishi. 20 Katika kipindi chijha Musa wadabadwa, wadali wabwino pachogolo pa Mulungu, wadaleledwa miezi itatu katika nyumba ya baba wake. 21 Nyengo wadataidwa binti wa Farao wadamtenga wadamlela ngati mwana wake. 22 Musa wadayaluzidwa mayaluzo yonche ya Kimisri, idali ndi mphavu katika mau ndi vichito. 23 Nampho pamalo pakutimiza vyaka arobaini idamjela katika mmitima mwake kwaendela abale wake, wana Akuisraeli. 24 Yapowadamwona Mwisraeli niwachitidwa voipa Musa adamuimila utikulipiza kisasi uyowadali wamamuu amuonela kwa kumbula Mmisri. 25 Wamaganizila kuti abale wake siajiwe kuti Mulungu wamlamiecha kwa janja lake nampho siamajiwe. 26 Siku limachata wadapita kwa baadhi ya Waisraeli anyiyao adali amayambana wadaesa kwagwilichana wadakamba anyabwana anyiimwe ni mabale mbona mlakwilana anyaimwe kula anyaimwe? 27 Nampho uyowadamlakwila jirani wake wadamsukumila kwa kutali ndikukamba yani wakuchita mtawala ndi muhumu watu? 28 Iwe ufuna kunipa ngati umowampela mmisri julo?'' 29 Musa wadatawa baada yakuvela chimwecho wadali mlendo katka jiko la Midiani ambapo wadali baba wa wana awili. 30 Baada ya nyaka arobaini kupita malaika wadamchokela katika jangwa lamapili Sinai katka mwala wa moto mkati mwa matengo. 31 Nyengo Musa yapowapena moto wadazizwa ndi kustajabu chija wadachiona ndi yapowaesa kuchisendelela ili kuchipenya sauti ya Bwana idamjela idakamba. 32 Ine ni Mulungu wa mababa zanu Mulungu wa Abrahamu ndi wa Isaka ndi wa Yakobo. Musa wadatentemela ndi siwadasutu kupenya. 33 Ambuye adamkambila, "vula vilato pamalo yapo waimani. 34 Naona mazunjo ya wantu wanga alipo kumisri navela kudwala kwao nane nachika ili nalamiche ehipano maja nikutume iwekumisri.' 35 Uyu Musa ambae wadamkana, nyengo yapoadakamba, yani wakuchita kukala mtawala ndi olamua watu? Wadali ndie ambae Mulungu wadamtuma wakale mtawala ndi mkombozi. Mulungu wadamtuma kwa janja la malamulo ambapo wadachokela Musa mtengo. 36 Musa wadamchogoza kuchoka Kumisri baada ya kuchitamiujiza ndi alama katika Misri ndikatika nyanja ya Shamu, ndi katika jangwa kwa ntawi ya vyaka arobaini. 37 Ni Musa uyu nde uyo wadakambila wantu wa Kuisraeli kuti, Mulungu siwakuinulieni nabii kuchokela pakati pa mabale wanu, nabii ngati ine.' 38 Uyu ni munthu ambae wadali katika msonkhano jangwani ndi malaika ambae wadanena nae katika phili Sinai, uyu nde munthu ambae wadalandila mau ilolidali la moyo ndi kutipacha ife. 39 Uyu ni munthu ambae baba watu adakana kumvechela, adamsukumila kwakutali ndi katika mitima yao adan'anamukila Kumisri. 40 Katika kipindi ichimene adamkambila Haruni tikonjele visanamu ivositichogoze, huyu Musa uyoadali wamatichogoza kuchoka kuchoka katika jiko la Misri, sitijiwa ichochidampeza.' 41 Chimwecho adakonja ndama kwasiku izi ndiadachocha mayamiko kwa chimwecho chosepa ndi adasangalala kwa chifuko cha nchito za manja yao. 42 Nampho Mulungu wadang'anamukila ndi kwapacha aabudu utondwa za kumwamba, ngati umoidalembedwa kuchitabu cha manabii, bwa mwanichochela ine mayamiko ya wanyama yaomwachinja kujangwani kwa ntyawi ya vyaka arobaini nyumba ya Israeli? 43 Mwavomela hema ya kukutania ya maloke ndi ntondwa ya Mulungu refani, ndi picha iyomdaikonja ndi kuabudu wao, ndi sinapeke kwakutali zaidi ya Babeli.' 44 Baba watu adali ndi hema la kukomanilana la hushuhuda, ngati Mulungu umowadalamulila yapowadakamba ndi Musa, kuti wadaikonja kwa mfano wauja uowauona. 45 Ili ni hema ambalo baba watu, kwa nyengo yao adapelekedwa katika jiko ndi Joshua. Ili idachokela chimeue hadi siku za Daudi. 46 Ambae wadapata kubali pamaso pa Mulungu, ndi wapempha kufuna makao makuu kwa Mulungu wa Yakobo. 47 Nampho Seleman wadammangila nyumba ya Mulungu. 48 Ata chimwecho wali kumwamba siwakala mnyumba izozamangidwa kkwa manja, ii ngati nabii umowadakambila. 49 Kumwamba ni mpango wanga wa ezi, ndi dunia ni sehemu yakuika myendo yanga, nyumba yaiyanji simunimangile? Wakamba Ambuye, Au kuti pamalo panga pomulila? 50 Osati janja langa laichita ivinthu vonche?' 51 Anyiimwe wantu mwene kosi lolimba anyiyao sadatailidwe mmitima ndi mmasikio, kila nyengo mumtimba Roho Oela, mchita ngati baba wanu umoadachita. 52 Anyaimwe wantu mwaandila shelia ija yaagizidwa ndi malaika nampho simdaigwile. 53 Ni nabii wanji katika manabii ambae baba wanu siadamtese? Adaapa manabii onche adachokela kabla ya ujio wa mmoji ali ni hoki. Ndi chipano muli osati ndi akupa wake pia.'' 54 Potela ajumbe abalaza yapoadavela adapwetekedwa mmitima mwao adamsagila mano Stefano. 55 Nampho iye, ikakala wajala roho oela, wadapenya kumwamba kwa makini ndi waduona utukufu wa Mulungu, ndi kumuona Yesu waima janja lakuume la Mulungu. 56 Stefano wadakamba,"penya naiona mbingu zavinikilidwa, ndi mwana wa Adamu waima janja la klia la Mulungu." 57 Nampho wajumbe wa baraza adatimba kelele kwa sauti za amwamba adaziba masikio yao, adamtamangila kwa pamoji, 58 adamtaya kubwalo kwa jiko adambula myala, ndi mashahidi adavula nchalu zao kubwalo ndi kuika panchi pafupi ndi myendo yamyamata uyo wamatanidwa Sauli. 59 Ayapo adali nambula myala Stephano wadaendelea kumtana Ambuye ndi kukamba, "Ambuye Yesu mlandile roho yanga." 60 Wadapiga magoti ndi kutana kwa sauti yaikulu, "Ambuye siudawelengela dhambi ii." Yapo wakamba yaya, wadadadula roho.

Chapter 8

1 Sauli wadali pamavomelezana ya nyifa yake, siku limenelo nde wadsayamba kwa zunja kinyume cha kanisa lidali Kuyerusalemu. Ni okulupalila onche anyiyao adachoka katika makamu ya Yudea ni Samaria, ila osati ni otumidwa. 2 Wanthu akumjiwa Mulungu adamzika Stefano ni kuita maombolezedwe Yakulu juu yake. 3 Nampho Sauli wadaliwananga kupunda kanisa. Wadapita nyumba kwa nyumba ni kuwaburuza kubwalo wachikazi ni wachimuna, ni kwa taifa madende. 4 Okulupalila anyiyao adali achokachoka adali akali kulilakilila mau. 5 Filipo wadachika katika muji wa Samaria ni wadamtangaza Mpulumusi kumeneko. 6 Baada ya wanthu kuvela ni kupenya mambo wachita Filipo, adaika kujipenyelela juu ya chija wadachikamba. 7 Kuchoka pamenepo wanthu ambili anyujao adavela, mzim oipa udawachoa wanthu uku alila kwa sauti yaikulu, ni ambili adakosa nkhongono ni asaende adapulumuchidwa. 8 Ni kudali ni chisangalalo chachikulu katika muji. 9 Nampho padali ni munthu mmojhi katika muji uja jnina lake Simoni, uyo wadali wamachita ufiti, ambao wadautumia kwadbwaicha wanthu akamula Samaria, nthawi wamakamba kuti iye ni munthu ofunika. 10 Wasamaria onche, tangu wamng'ono hadi wamkulu, adamvechela adakamba, "munthu uyu ni ija nkhongono ya Mulungu ambayo ni yaikulu." 11 Adamvechela, chafuko wadazizwicha muda wautali kwa ufili wake. 12 Nampho, nthawi akulupalila kuti Filipo wadalalikila juu ya ufumu waMulungu ni juu ya jina la Mpulumusi, adabatizidwa, wachimu kwa wachikazi. 13 Ni Simoni mwene wadaklupalila. Baada ya kubatizidwa, wadaendekela kukala ni Filipo, yapo wadaona langizo ni vodabicha vimachitika, wadadabwa. 14 Nthawi otumidwa Akuyerusalemu yapo adavela kuti Samaria yalandila mau la Mlungu, wadatuma Petro ni Yohana. 15 Nthawi yapo adaliachika wadapemphela, kuti aulandile mzimu oyela. 16 Mpaka muda umeneo, mzimu oyela udali ukali usachikile ata mmoji wao, adali tu abatizidwa uwajina la Ambuye Mpulumusi. 17 Ndipo Petro ni Yohana wadaikila manja ni otumikila, wadafune kwapacha ndalama. 18 Nthawi Simoni yapo wadaona kuti mzimu oyela wachochedwa kupitila kuikidwila manja ni otumikila, wadafuna kwapacha ndalame. 19 Wadakamba , "nipacheni ii nkhongono, dala kila uyo sinimulikile manja walandile mzimu oyela." 20 Nampho Petro wadamkambila nalama yako pamoji ni iwe visowela ktyali, kwa ndande waganiza kuti karama ya Mulungu ipatikane kwa ndalama. 21 Lilibe malo katikachinthu ichi, kwa ndande mtima wako siuli wa bwino pamasa pa mlungu. 22 Chimweeho basi lapa voipa vako ri kumpempho mlungu pina ulekeleledwe magamizo ya myime walio. 23 Chafuko mona uli katika kupachidwa voipa ni kumangidwa chimo. 24 simoni wadayomkhe nikukamba mpempheni ambuye kwa ndonde yanga pakuti mambo yonohha mwayakamba yakoza kumchokela. 25 Nthawi Petro ni Yohane yapo adali kupenya ni kulalikila mau la Ambuye adabwela Kuyerusalemu kwa njila imeneyo adalikila mau katika vijiji vambili va Wasamaria. 26 basi angelo wa ambuye adanena ni filipo ni kukamba mulika ni upite kusini katika njila ipita pomehh Payerusalemu kupita kugaza (njila iyi katika palulu). 27 Wadamulikani kupeta pene kudali ni munthu wa Kuethiopia wali ni malamulo yakulu pomehi pakondase maluia wa Kuethiopia waikidwa pamwamba viirithu vake vonche nae wadali wazipita Kuyerusalemu kupempha. 28 Wadali mwazifika wakalamgali wasoma chikala cha mlose Isaya. 29 Chimwechi Filipo wadatamanga liwilo wadamvela niwasoma katika chikalakala cha mlose Isaya wadakamba bwani ujiwa icho uchisoma. 30 Muethiopia wadakamba sinikoze bwanji munthu yapo siwaminichogiza wadampempha Filipo wakwele gani ni nukala pamoji naye. 31 Mzimu wadakamba ni Filipo, "sendela pafupi ni gari ili ukagwilizane nalo. 32 Chapamo fungu la malembo ilo wamaliosoma muethu pia ni ii wadachogozedwa ngati mbelele kupita kumachinoni ni kuchinjidwa ningali mbelele wadakala chete wada masule mndomo wake. 33 Kwa kusikitichidwa kwake lamulo lake lidachochedwa yani siwakombile obadwane wake? Maisha yake yachochedwa katika jiko.'' 34 Basi buluda wadamfunchha Filipo ni kukamba nikupempempha ni mlose yali uyo wakambidwa ninha ni la Isaya kumtangazila nihani za Mpulumusi . 35 Ali mnjila, adafika pali maji, Buluda wadakamba, "penya, pali maji kumtangazila nkhani za Mpulumusi." 36 Ali mnjila adafika palimaji buluda wadakamba penye pali maji yapa chiani chizwea usisabatizidwa? 37 Mau yaya"chimwecho Muethiopia wadayamkha "nikulupalila kati Mpulumusi ni mwona wa Mlungu wadalamula gari liimikidwa. 38 Adapila mkati mwa maji pamoji ni Filipo ni buluda Filipo wadambatiza. 39 Nthawi achoka muja mmaji mzimu wa Ambuye udampeleka Filipo kutali buluda wadamuona wadapita nyile yake washangelia. 40 Nampho Filipo wadachokela Kuazoto wadapita katika mkoa uje ni kulaikila mau katika miji yonchhe mpaka yapowadayika Kukaisaria.

Chapter 9

1 Nampho Sauli wadaendekela kukamba votisha atavakupedwa kwa opuzila wa Ambuye, wadapita kwa wamkulu wa nchembe. 2 Ndi kumphempha barua ndande ya makanisa kumeneko Kudameski, il kuti wakampata munthu uyo wali mkati mwa njila imeneyo, wakale wamuna au wamkazi, wamange ndi kwaapeleka Kuyerusalemu. 3 Ata yapo wadali pasafari, idachokela kuti yapowadakalibia Kudameski, ghafla idamwakila konche konche dangalila kuchoka kumwamba. 4 Nayo wadagwa panji ndi wadavela sauti ndiikamila, "Sauli, Sauli, mbona unitesa ine?" 5 Sauli wadajibu panji ndi wadavela sauti ndii kambila Sauli mbona unitesa ine? 6 Nampho ima lowa kumjini nawe siukambilidwe yayo ifunikana uchite. 7 Anjiwaji wanthu adili paulonda pamaji ndi Sauli adakala kacheta ndiavechela Sauli asidaona muthu. 8 Sauli wadainuka panchi ndi yapowada masula mado yake siwadakoze kuona chinthu adamgwila janja adampeleka mpaka Kudameski. 9 Kwa siku litatu siwapena siwakumwa. 10 Ndo kudali ndi opuzila Kudameski jina lake Anania Ambuye adakamba naye pakatipa kuleso amana ndi wadakamba penya ndilipana mbuye. 11 Ambuye adakambila muka ulipakati pa mtaa utari nidwa Nyofu ndi mkati mwa nyumba ya Yuda ndi uka funchile munthu kuchaka Tarso watani dwa Sauli pakuti penya watopempha. 12 Ndi wadamwona pakati pa kulesa muthu jina lake Anania ndi walowa ndi kumwiikila maja pamwamba pake ili kuti wapate kupenya. 13 Nampho Anania wadajibu Ambuye navela habari za munthu uyu kwa wanthu ambili kwa namna yaji umawachitila voipa oyela akumeneka Kuyelusalemu. 14 Yapa wali ndi malamulo kuchoka kwa wakulu anchhombe kumgwila kila mmoji uyowalitana jina lako. 15 Nampho Ambuye adamkambila mapita pakuti iye ndi chombo cha chagulidwa kwanga walitenge jino langa pachoolo pa pajiko ndi ofumu ndi wana wa Israeli. 16 Pakuti sinalangize umo vili vambili ivovidi kutesedwa ndande ya jina langa.'' 17 Anania wa dapita wadalewa muja mnyumba wa damuikila manja wadakamba m'bale Sauli Ambuye Yesu yao adakuchokela pati panjilazapo umoja ani tuma upata kuonancha ndi ujazidwe Mzimu Oyela. 18 Ghafla vidagwa pamaso pake vinthu ngati magamba wadapata kuona wadaima wadabatizidwa wadadya chakya ndi wadapata mphavu. 19 Wadakala pamoji ndi opuzila kumeneka Kudameski kwa siku za mbili. 20 Nyenga imeneyo wadamtangaza Yesu mkati mwa makanisa wadakamba kuti iye ndi mwana wa Mulungu. 21 Ndi anche davela adashangaa ndi kukamba asati munthu uyu eyawada wawananga anche adali tana jina ili kumeneka Kuyerusalemu ndi yapowadali kwa chifukwa cha kwaamanga ndi kwapeleka kwa wakulu anchembe. 22 Nampho sauli wadachitichidwa kutangaza ndi kwa hiti Wayahudi anyiya amakala Kudameski achanganyikawe ndi kusibitisha kuti uyu ndi Kristo. 23 Baada ya siku lambili Wayahudi adachita maganizo pamaji ili amusipe. 24 Nampho mpango wao udajuulikana ndi Sauli adamvizia pakamo usana ndi usiku apte kumuipa. 25 Nampho apuzila wake adamtenga usiku adamchicha kupitila muukuta adamchicha panchi mkati mwa chikapu. 26 Ndi Sauli zapowadafika Yelusalemu wadaesa kujiunga ndi apuzila nampho amata muapa siamakulupalile kutinaye ndi apuzila. 27 Nampho Barnaba wadamtenga ndi kmpeleka kwa atumiki ndi adaafo takalela jinsi Sauli umawadamwanila mbuye panjila ndi mbuye umawadakamba ne ndi jinsi Sauli uma wa tandaula kwa ujasili kwa jina la Ambuye Yesu kumeneko Kudameski. 28 Wadapezana naa yapoadalowa ndi kuchoka Kuyelusalemu wadakamba kwa jina la Ambuya Yesu. 29 Ndi wafotokazi ndi Wayahudi Akiyunani nampho adaesa nyenga kwa kumupi. 30 Nyinga abale yapoadaji wa chinthu chimencha adamtenga mpaka Kukaisaria ndi ampeleke wapite ku Tarso. 31 Ndi yapokamisa lonche pakati pa Wayahudi Galilaya ndi Samaria lidali ndi mtendele ndi lidajangadwa ndi kuenda mkati mwa kumwuopa Mbuye ndi ufuru wa Mzimu Oyela kanisa lidakula kaongezaka idadi. 32 Ndiyapo idachakokela Petro yapo wamazungukazunguka bendeka zonche za mkaa wadaachikilila waumini aisha mkati mwa maji wa Lida. 33 Wadamuona kumeneko munthu mmoji jina lake Ainea munthu mmeneya wadati patitanda vyaka nane pakuti wadapeoza. 34 Petro wademkambila Ainea Yesu Kristo wakulamiche ukali ndi ujiyalile chitanda chako mala wadauka. 35 Ndi wanthu oncha amakala kulinda shareni yapo adamuena munthu uyu adamng'anamukila Mbuye. 36 Padali ndi opuzila Kuyafa watanidwa Tabitha ila lidatafsilidwa Dorcas uyu wamkazi wadajala nchita yabwina ndi vichito va kulekelela yaye wadachita kwa asauka. 37 Idachokela pakati pasiku zimenezo wadadwala ndi wadafa yapoadamsafirisha adamkeza chumba cha pamwamba ndi kumgeneka. 38 Pakuti lida kalibu ndi Yafa ndi epulila adavela kuti Petro wadali kumeneka adaatuma wanthu awili kwake adampempha uje kwatupi kuchedwa. 39 Petro wadauka ndi kuchoka pamoji nao yapoawafika ndampeleka mkati mwa chumba cha pamwamba ndi ofedwa ndadwa ndachamunaa adaima karibu naye ndialila ndi amlangiza koti ndi nchalu izo Dorcas wadasakela nyengo walipamoji nao. 40 Petro wadaa cha enche kubwala kwa chumba wada gwada magoti wadapempha ndeyapo wadangana mukila ntupi wadakamba Tabitha ukawadamasula maso yake ndi wadamwona Petro wadakala panchi. 41 Nde yapo Petro wadamninkha jacha lake wanamwimika ndi yapo wadaafanaokulupalila ndi efedwa ndi achamu nao wadakabidhi kwao wali ndi umoye. 42 Chindu ichu chidajulikana kuyafa konche ndi wanthu ambili adamkulupalila mbuye. 43 Idachokela Petro wadakala siku zambili Kuyafa pamoja ndi munthu watanidwa simeni akonja vikwetu.

Chapter 10

1 Wadalipo munthu mwina wa mmujhi wa Kaisaria jhina lake amamtana Kornelio wadali wa mkulu wa asili kali Waaroma. 2 wadali munthu wamaphemphero ndi kukulupalila Mulungu iye ndi amnyumba mwake onche wamachocha ndalama zambili kwa Ayahudi ndi; ndi kumphempha Mulungu masikuli yonche . 3 Ntawi ya 3:00 usana wadaona vinthu mmaso mphenya angelo Amlungu amjela, angelo wadamkambila Kornelio. 4 Kornelio wadamphenya angelo ndi wadali ndi mantha kupunda ndi kunena ichi ndi chiyani mkulu angelo wadamkambila maphemphelo yako ndi mphotilio zako kwa osauka vakwela kumwamba ngati kumbukilo pamaso pa Mulungu. 5 Chipano tumiza wanthu kupita ku mujhi wa Yafa akaje ndi munthu mmojhi watanidwa Simoni iyeyo watanidwancho Petro. 6 Wakala ndi mkonja vikwetu watanidwa Simoni iye nyumba yake ili mphepete mwa nyanja.'' 7 Pambuyo pa angelo wamakamba naye kuchoka, Kornelio wadaatana anchito wake awili amnyumba mwake,ndi msikali wadali omphembeza Mulungu pakati pa asilikali amamtumikila. 8 Kornelio wadaakambila vonche vidamchokela ndi wadaatuma Kuyafa. 9 siku lidachatila alimnjila nthawi ya 12:00 ndi alipafupi ndi mujhi, Petro wadakwela kudale kukaphempha. 10 Ndi wadali ndi njala wamafuna chinthu kati wadye, nampho wanthu yapo amaphika chakudya, wadalangizidwa mmasomphenya. 11 Wadaona kumwamba kwa masuka ndichombo chichikha ndi chinthu china ngati nchalu yaikulu idachika panchi pa doti ndi visangwa vake vonche vinai. 12 Mkati mwake mudali zinyama za mitundumitundu amiyendo inai ndi zokwawa pa doti ndi visongwa pa doti, ndi mbalame za mulengalenga. 13 Ndi yadaveka mau kwaiye ''uka Petro iphandi udye, 14 nampho Petro wadakamba, osati chimwecho Ambuye ndande sindidadye chinthu chilichonche cho nyansa ndi chasayera. 15 nampho mau yadajhancho kaka wili, icho chayelechedwa ndi Mulungu usa chitana chonyansa. 16 Ichi chidaoneka katatu, ndichijha chombo chidakwelancho kumwamba. 17 Petro wali mkati mosokanizika pakati pa yajha wadaona mmasomphenya yatandauza chiyani, ona, wanthu anyiyao adatumidwa ndi Kornelio adaima pachogolo pa chicheko, adafunchila njila yopita kungumba 18 Ndi adaona ndi kufuncha ngati Simoni uyo wamatanidwanche Petro wakala paja. 19 Nthawi imeneyo Petro wamaganiza pakati zija za mmasomphenya Mzimu udakamba naye ona wanthu atatu akafunafuna. 20 Ukandi uchike upanchindi ujipita nawo usaopa nawa ndande inendatumidwa. 21 Petro wadanchi ndikunena inendeyija mumfunafuna ndande chiya ni mwaja?'' 22 Adakamba mkuu mmojhi jhina lake Komelio ndimuthu olungamandiwakonda mamphmphelo ndi wanthu amkumba bwino jhiko lonche la ayatudi wakambidwa ndimngelo wa mlungu kukutuma kuti upite kunyumba yake kuti wavele utenga kuchokila kwaiwe. 23 Petro wadaalandila mnyumba ndikukala pamojhi ndiiye umawa udachatila wadaukandi kupita nawo ndi mabale ochepa kuchokela Kuyafa adachana naye. 24 siku lidachatila adafika kukaisaria ndi Kornelio wadali walindilila ndi wadaatana pamojhi mabale wake ndimabwenji lake apafupi. Nyengo Peturo wadamuimika ndi kunena ine nane ndimunthu . 25 Nyengo Peturo walowa mnyumba Kornelio wadamlandila ndi kukwatama makana panchi mmyendo mwake pakumlemeka. 26 Nampho Peturo wadamuimika ndikunena ine nane ndi munthu.'' 27 Peturo nyengo ndiwamba naye wadalowa mnyumba ndiwakwama wanthu asonkhanikana pamojhi. 28 wadakambila anyamwe mjhiwa kuti osati lamulo la Chiyahudi kugwili zana kupina kuendeledwa ndi munthu uyo osati wa mtundu wanu namho Mulungu wandiza ine sindifunika kumtana munthu waliyencho kuti wonyanya kapina wosayera. 29 Nde mate yake ndinda popande mtafu yapo ndidatumidwa chifukwa chaizo kwaichi ndikuncheni ndanda chiyani mdatumidwa ndande yaine.'' 30 Kornelio wadakamba masiku yanai yapita nthawi ngati ino ndimaphemphera nyengo ya 3:00 usana mkati mwanyumba nyengo pachogolo panga ndidaona munthu aima wavala vivolo voyera. 31 Wadandikabila Kornelio mphemphelo yako yaveka pamaso pa Mulungu ndi mphoto zako kwa osauka zakala ukilo pamso pa Mulungu. 32 kwaicho tumiza munthu Kuyafa wakamtane munthu mmojhi uyo watanidwa Simoni waje kwaiwe uyo watanidwancho Peturo uyo wakala kwa munthu wakonja vikwetu mmojhi wtaamidwa Simoni uyo nyumba yake ili mphepete mwa nyanja. 33 Penyelelani milele uwu iye yaposiwajhe siwakambe ndi anyaimwe mulijemo mmalembo aja kale. 34 Peturo wdamasula pakamwa pake ndi kukamba zenedi ndaona kuti mlungu walinje lusankho. 35 Pambuyo pake kila mtundu munthu aliyonche waphemphera Mulungu ndikuchita vichito va bwino wavomeleka kwaiye. 36 Ujhiwa utenga uo wadauchocha kuchokela kwa wanth Akuisrael yapo wamalengeza nkhani za mtendele kupitila Yesu Kristo uyo wali Mbuye wataonche. 37 Mwachinawene wakumjhiwa icho chidachokela Kuyudea yonche ndichidayambila Kugalilaya pambuyo pa ubatizo uwo Yohana wadalengeza. 38 Izi zimamkuza Yesu Kristo Mulungu umo wadamtilila mafuta pa Mzimu Oyera ndi kwa mphamvu wadapita kuchita vabwino ndi kulamicha onche amachauchika ndisatuna pakuti mlungu wadali pamojhi ndiiye. 39 Ife ndi amboni pa vinthu vonche ivowadachita mmaiko ya Uyahudi ndi Kuyerusalemu uyu Yesu uyo adampha ndi kumwamba pa mtanda. 40 Uyu munthu wadamucha siku la katatu ndikumchita kujiwikana. 41 Osati kwa wanthu onche nampho kwa mambo ni yawo adasakhidwa Mulungu chiyambiepo ife tachinawene timadya naye ndi kumwa naye pambuyo pochidwa kuchokela kwa akufa . 42 watilamula kulalikila kwa wanthu ndiku tilila umboni uyu ndiye mlungu wadamsankha kukhala olamulika wanyi yaoaliamoyo ndi yao afa. 43 Pakati payiye alosi wanche atile umboni kuti uyo wakulupalila waliyonche mkati mwaiye siwakululukidwe machimo kupitila jhina lake.'' 44 Nyengo Petro wamandekela kakamba Mzimu Oyera udaa chikila onche yao amavechela utenga wake. 45 Wanthu wajha adagwilana ndi gulu lokulupalila aumbalidwa onche adaja ndi Petro adadabwa chifukwa cha mphaso ya Mzimu Oyera uyo wadamwazidwa kwa wanthu amaika oyera uyo wadamwazidwa kwa wanthu amaiko. 46 Pakuti adavela anyiyawao amaiko akamba mikambo injake ndi kumphemphela Mulungu Petro wadayankha. 47 Walipo munthu waliyenche wakoza kucheleza mmojhi kuti wanthu oyera ngati ife. 48 Ndeyapo wadaiamula kuti abatizidwe mjhina la Yesu Kristo pambuyo adampempha wakale nao masiku yakuti.

Chapter 11

1 Akumwa ndi abale waja adali ka Yuda adaniva kati ametundu adalandila maua ni Mulungu. 2 Pamene Petro adabwela Kuyelusalemu gulula wanthu ochelidw aadakangana nayo adakamba uti, 3 ''Wemvina ndi wanthu asadulidwa ndi kudya nazeo pamoji.'' 4 Nampho Petro adayamba kukamba vimene vedamchikitila kwa aliyentche. 5 Nidali kupemphera kamji wa yopa ndedaona masomphenya chotengela chikusika kuchokela kumwamba ngati chisalu chongilandwa nichonga zake zinayichidatichika pedali ine. 6 Nidachipenyetchake ndi kuchiganizila nedepenya nyama za mayendo inayi ni vilombo va pajiko la pentche ni vokwawa ni mbolame amlengalenga. 7 Nevala mau okamba ndi ime akuti Petro ukayepha ni udye. 8 Koma nidati iyayi Ambuye sunenadije kanthu kalikonche koepa kapena kosakanjeka sekadelewa mtanizo mwanga nikale lomwe. 9 Koma mau anabwelantche kuchokela kumwamba yicho Mulungu wa chiyeletcha usachetae chakada. 10 Yachi chidachitichwa katatu pambuyo pake chidatengechwa kupite kumwimba 11 Tapenyani nthawi yomwe wanthu ustahi adaima pabwalo pa nyumba iyo tedalimo adatumuedwa kukaiseke kubwela kwa ine. 12 Ngumu udanikwambela kuti nepite nawo osalekanit cha nwo ndi wenthu sita adanipelekaga uleplapitaka nyumba ya munthu wine. 13 Adatikambila umo udamuonela malaika adayemila mteti ni wa nyumba nikakamba lumani wanthu kuyopa akamutenga Simoni otanidwa Petro. 14 Agakemba ujumbe kwa mwe umene ugaombela ni abali wako ontche.'' 15 Pamene nidayamba kukamba nawo Mzimu Oyela anabwela pamwamba pawo ngati mene adabwela pa ife poyamba paja. 16 Nikubuka maze Ambuye adakamba Yohane adawabatiza ndi maji, koma yizafika nthawa yomene muzabatizadwa ndo Mzimu Oyela.'' 17 Ndithu ngati Mulungu wachotcha zawadi ngati adetipatche ife panene tidakhupilila Ambuye Yesu kristo ine ndani kuti kumpinga Mulungu? 18 Pamene adavela zimenezi adakhala Mulungu ndikukamba Mulungu wapeleka kulapa ngakhala kwa anutunefu.'' 19 Basi okhulupilila mazunjo yadayamba pamene Stefano adaphedwa ndifo adasalana kwinakwa na Kuyelusalemu akhulupilila adapila kutari kufomuke kipolo mpakana ku Antiokia. Adakamba uthenga ohusu Yesu Kristo yekha basi kwa Ayuda osati kwa aliyentche. 20 Koma mbali ya wina ni wanthu ochokela ku Kipro ndi Krene, adabwela Antiokia ndi kukamba Wayunani ndi kukalika za Ambuye Yesu. 21 Nizanja la Ambuye lidali pamoji ndi tuu, ndi zanthu ambili adakhulupilila ndi ang'anamuka Ambuye. 22 Ndi nkhani zao zidafika mmakutu mwa kanisa lonche la Kuyerusalemu, ndi adamtuma Barnaba apite mpakana ku Antiokia. 23 Yapo adafika nikuona mphanile Mulungu adakondwa kwambili, adakulimbikitcha onche kukhala ndi Ambuye m'mtima wawo. 24 Chifuwa adali munthu wabwino ndi adajazidwa ndi Mzimu Oyela ndi chikhulupilil ni anthu ambili adaonjezeka kwa Ambuye. 25 Pambuyo Barnaba adapita Kutariso kukamuona Sauli. 26 Yapo adamupheza, adabwelanayo Antiokia. Yidali chaka chatunthu, adabwela pamoji ndi kanisa lidephungasa wanthu ambili. Ndi ophunzila adatanidwa Akristo koyamba ku Antiokia. 27 Ni panthawi yameneyo wanafunzi kapena olosa ambili adabwela ku Yerusalemu mpakana ku Antiokia. 28 Mmoji wao ndi Agabo nde jina lake, wada adafina nde mphamitu ya Mzimu Woyela adalosa kuti pazakhela njala yejikulu pajiko lontche lapasi njaleyo yidabweladi pa nyongo yake ya Klaudio. 29 Pamenepo Akristo aja akhulupilila kutumuza thandizo kwa abale okhala ku Yudea, kuti aleyontche atumize molingana ndi kupata kwake. 30 Zimenezi zidachitikadi, adatuma Banabasi ndi Saulo, kukapelika thandizolo kwa akulu amphingo.

Chapter 12

1 Ntawi, imeneyo fulo Helode wadalangiza jauja lake kwa ochepa nche ome anchokela mkati thagulu dala apeze mavuto. 2 Wadamopa Yakobo mbalewake Yohana kwa chikwanje. 3 Pambuyo pakupeuya kuti iwakadwila Wayahudi wadamgwila ndi Petro loncho liidali ntawi ya mikate yo chuchuluka. 4 Yapo adamgwira adamwika mndende ndi adaika maguru yanai askari dalakuti kumpenyelela wama kurupalila kumpeleka kwawantu pambuyo pa Pasaka. 5 petro wadailadwa mdende nampo mapeupelo yadachifidwa kwa mpavu ndigulo ndande yaiye kwa mrungu. 6 Siku wakarli herode osapifa kumcho cha usiku omweo Petro wadali wan'gona pakatikafi pa azankongo awili ukuwamangidwa ndi vingwe viwili ndialonde alipa chogoro pachicheko ukundi ndi alipenyelela ndende. 7 Peuyawi malaika wa Mulungu mwazizili wadachokela ndi dangalila mkati wada mwenya Petro mmbalati ndi kumuucha ndiwakamba, ''uka msanga nde pamenepo vingwe wadamangidwila vida masuka kuchokela mmanja mwake." 8 Angelo wadamnenela ''valancharo zako ndivilato vako'' Petro wadechifa chimwencho angelo wademkambila vala chovala chako undichate.'' 9 Mmwemo Petro wada mchata angelo ndiko choka kubwalo, siwada ziudikile chimeve chifa chitidwa ndiangelo ngati chazene wamaganize waona ndoto. 10 Pambuyo pakupyeuka pa ulinda oyamba ndipaka wili atafika pachicheko cha chichuro cholowela kupita mkati mwamuji chidamasuka chene chifuko chao adachoka kubwalo adachika mopifa kenake angelo wadamsia. 11 Petro yapo wadafifiwa wadakamba'' chapamo nda vawanazo kutimulungo wadamtuma angelo wake dala kundi chocha nikati mwa mauja ya Herode ndikwazofunikila za wantu woche wa Kuuyahudi.'' 12 Pambuyo poyajiwa yaya wadaja mnyumba ja Mariam majiwake Yohana mmene wali Marko wantu a Mulungu ambili adakalila limoji ndiapempela. 13 Pamene wadawodika pachicheko choka rizidwa mtumiki mmoji wamkazi wa damidwa lode wadaja kummasula. 14 Yapo wadejiwa kuti mau ya Petro kwa chisangalalo wadepela kumasula chicheko pambuyo pake wadatawila mkati mwachipinda, ndi kwa ajiwiche kuti Petro waime pachogoro pa chicheko. 15 Mmwemo adakamba kwaiye, "iwe ndi ubwabwazika" napo wadalangiza maso kuti iyedi adakamba, "mmeneyo ni angelo wake." 16 Nampho Petro wadaendekela kumasura chicheko yapo adamasula chicheko adamuona ndi adazizwa kupunda Petro wadaakambila akale kachete mwa janja. kachete kachete ndi wadaakambila mmene Mulungu wamchochela mudende wakamba, 17 "Akambileni nkani izi Yakobo ndi abale wake, "pambuyo wadachoka ndi kupita malo yena. 18 Yapo idari usana kudali ndi madandaulo kupunda pakati pa alonda kuchokela chimene chachokela kwa Petro. 19 Pambuyo pa Herode yapo wadamfuna ndi oamuona wadaafuncha alonda ndi kuchocha lamulo kuti apedwe wadapita kuchokela ku Uyahudi mpaka ku Kaisaria ndi kukala kumeneko. 20 Herode wadali ndimpwai pamwama pa wanthu atilo ndi Sidoni adapita kwa umoji wao kwaiye adakala ndi ubwenji ndi brasto otandaza wake wamkuru wajiko dala kuti waatadize potela pake adapempa mtendele chifukwa jiko lao lidalandila chakudya kuchokela jiko la wamkuru wa jiko. 21 Siku lidaganizilidwa Herode wadavala nchalu za ulamulilo ndi kukala pampando wake wa mkuru wa jiko ndi kwaakambila. 22 Wanthu adamenya mapokoso, "Yaya ndi mau ya Mulungu osati ya wantu!" 23 Mwa zizizi angelowadammenya, chifukwa siwadampache Mulungu ufuru wadajedwa ndi mkango ndi wadamwalila 24 Nampo mau la Mulungu lidakula ndi kumwazika. 25 Pambuyo pa Barnaba ndi Sauli kumalizila chitandizo chao adachoka pamenepo kubwelela ku Yerusalemu adamtenga Yohana mmene jina lake la kubadwa ni Marko.

Chapter 13

1 Chipano pa kanisa la Antiokia padali ndi wena wa olosa ndi oyaluza adali Barnaba Simeoni (wamatanidwa Nigeri) Lukio wa Kukirene (mbale wake osati wa mwazi wa Herode mchongozi wa mkoa) ndi Sauli. 2 Yaupa adali kulambila atate ndi kumanga mzimu oyela wadanena nipatulileni pambhepete Barnaba ndi Sauli, aichite njhito vyo natanila. 3 Pambuyo pa kanisa kumenja, kupembha ndi kuike manja yowo kumwa kwa wandhu yawa akasiya apite. 4 Kwa icho Barnaba ndi Sauli wadamlemekeza Mzimu Oyela ndi kuchika kupitila kuseleukia; kuchoka kumeneko adapitila mnyanja ya mchele kupitila kuchilumba cha Kipro. 5 Yapoadali pa mujhi wa Salami adalalikila mau la Mulungu pa masinagogi ya Wayahudi mmwemoncho adali pamojhi ndi Yohana Marko ngati otangatila wawo. 6 Yapoadapita pa chilumka chonche mpakana kupafo adapeza mundhu nnajhi mfiti Myahudi ohosa wa unami mmene jhina lake lidali Bar Yesu. 7 Mfiti uyu wadagwili zana ndi liwali Sergio Paulus uyowadeli mundhu wa njelu. Mundhu mmeneyo adalalika Barnaba ndi Sauli kwa ndanda adafuna kuvela mau la Mulungu. 8 Nampho elima '' yujha mriti'' (mmwemo ndimo jhina lake limado ngosoledwa) adawachucha; adayesa kumnganamula yujhe liwali achoke kuchikulupi. 9 Nampho Sauli uyowadatanidwa Paulo wadali wajhazidwa ndi Mzimu Oyela wadamcimikizila maso. 10 Nde anane ''iwe mwana wa chilombo wajhazidwa ndi mitundu yonche ya kunyenga ndi kwonda. iwe ni mdani wa kila ntundu wa malinga siusiya kuzinganamula njila za atate izo zaongoka bwanji siukoze? 11 Chipano penyani jhanja la tate lilipo pamwamba pako ndi siukale osapenya siuliona gehua lava nyengo ''mara kamojhi'' punduulu ndi mdima vidangwa pamwamba pa Elimas wadayamba kuzungulila pajha ndi wapembha wandhu amchogoze ka kumgwila jhanja. 12 Pambuyo pa liulali kupenya ichochachokela wakulupilila kwa ndande wadazizwachidwa kwa mayaluzo kukuza atate. 13 Chipano paulo ndi mabwenji wake adayende ulendo mmanji kuchokela kupafo ndi kufika kuperge pa pamfilia nampho Yohana adawasiya ndi kubwela kuyerusalemu. 14 Paulo ndi bwenji lake adayende ulendo kuchokela kuperge ndi kufika ku Antiokia ya pisidia kumeneko adapita pa sinagogi siku ya sabata ndi kukala panjhi. 15 Pambuyo pa kusoma malamulo ndi olosa achogoleli wa sinagogi adawatumazila utenga kunena Abale ngati mulinao utenga wa kutila mtima wandhu pano nenani.'' 16 Kwa icho Paulo wadaima ndi kupila Jhanja kunena wachimuna aku Israel ndi anyiimure irewe mvumeleza mlungu vechelani. 17 Mulungu wa anyiwaja wandhu wa Kuisraeli adewasagula anyatate wanu ndi kuchita wandhu ambili yapoadakala pa jhiko Kumisri, ndi kwa jhanja lake kukwezedwa adawachogolela kubwalo kwake. 18 Vyaka arobaini adadikilila pa pululu. 19 Pambuyo pa kuyawananga mayiko saba pa jhiko la Kukanaani adapacha waudhu watu jhiko lawo kwa kupachidwila. 20 Vochokela ivi vonche vidachokela kupunda pa vyaka mia nne ndi hamsini pambuyo pa vinthu ivi vonche Mulungu adawapacha olamula mpakana Samwel mlosi. 21 Pambuyo pa yaya wandhu adapembha mfumu mwemo Mulungu adapacha Sauli mwana wa Kishi mundhu wa kamu la Benjamini kukela ufumu kwa vyaka arobaini. 22 Ndipo pambuyo pa Mulungu kumchocha pa ufumu adamkweza Daudi mwana wa Yese kukala mfumu wawo idali ndi kukaza Daudi kufi Mulungu wadanena nampeza Daudi mwana wa Yese vukala mundu okondechedwa ndi mtima wangai uyo wasichite kila kandhu nichikondo.' 23 Kuchoka ku ukoo wa mundhu uyu Mulungu waipelekela Israel Mpulumuchi Yesu ngati umowadapanganila kuchita. 24 Limenelo lidayamba kuchokela mmbuyo mwa Yesu kujha Yohana payamba wadalalikila ubatizi wa kelapa volakwa kwa wandhu wonche wa kuIsrael. 25 Nayencho Yohana yapo wadali kumalizila njhito yake wadanenae mganizila Ine ndi yani? Ine osafi yujha nampho vechelani wakujha kumbayo kwanga sinifunika kumasula sabato za myendo yake.' 26 Abale wana wa kamu la Abrahamu ndi wajha yawo pakati panu mmulezi mekaza Mulungu ndi kwa chifuko chatu kuti kutenga uwe wa Chipulumuchi watumidwa. 27 Kwa anyiiwo akala Kuyerusalemu ndi wakwalamula wao siwadamzindikile kwa umo wali ndi poje siada uzindikile utenga wa olosa uwo usomedwa pa sabato; kwa icho adakwanilicha utenga wa olosa kwa kumlamula nyifa Yesu. 28 Ingikale siwadapate ndande ya bwino kwanyifa mkati mwake adampembha Pilato amphe. 29 Yapo adamaliza vocheta vomche vidalembedwa kukuza iye adamchicha kuchoka pamtego ndi kuungoneka mmanda. 30 Nampho Mulungu wadamhyucha kuchokela kwa akufa. 31 Wadaonekana kwa masiku ya mbili kwa anyiwajha adapita pamojhi ndiye kuchokela ku Galilaya kupitila Kuyerusalemu. Wandhu yawa chipano ndi amboni. 32 Mmwemo tikupelekelelani nkhani za owino kukuza vipangano adapachidwa achambuyatu. 33 Mulungu adaika vipangano ivi kwaife, wana wawo, pa limenelo adamhyusha Yesu ndi kumbwezancho pa umoyo. Ili nalo lidale mbendedwa pa Zaburi ya kawili; iwe ndi mwana wanga, lelo nakala atate wako. 34 Namponcho kukuza uzene ndi kuti adamhyucha kuchoka pa akufa kuti tuphi lake lisadawanangika, okamba chimwechi; "sinikupache kuyela ndi mwawi wazene wa Daudi' 35 Iyi ndiyo ndande kunena nancho p Zaburi yena, "siulamula oyela waiwe kuchiona choola.' 36 Pakuti pambuyo pa Daudi kutumikila chikondi cha Mulungu pa chibadwa chake, wadagona, wadagonekezedwa pamojhi ndi anyatate wake, ndi kuwena kuwanangika, 37 Nampho uyowahyushidwa ndi Mulungu siwadaone kuwanangika. 38 Mmwemo ndi ijhiweke kwa anyiimwe,abale, kupitila mundhu uyu, chilekelelo cha machimo. 39 Kwa iye wakulupalila wawelengeda malinga ndi vichito vonche ivo matauko ya Musa sidayakapatila malinga. 40 Mmwemo basi kalani ojhipenyelela kuti chindhu adachikambilila olosa sichidachokela kwa anyiimwe. 41 Penyani, anyiimwe mpepula, ndi kuzidwa mkawanangikidwe, kwa kuti mchita nchito masiku yanu, nchito iyo sinikoze, kuikulupalila atangati muudhu siwakufotokaozeni. Nyengo paulo ndi barnabe yapo adachoka wandhu adapenthe ake mbe mau yaya siku ya sabato ikujha.'' 42 Nyengo Paulo ndi Barnaba yapo adachoka, wandhu adapembhe akembe mau yaya siku ya sabato ikujha. 43 Nyengo nsoghano wa sinagogi yapoodata wajahudi ambili ndi opulumuka omiliha adawachata paulo ndi barrabe yawo atkambe nawo ndi kwa suimikuza aendekele pa neema ya mulungu. 44 Sabato iyoidachatila pafupi pa mujihi wa mphuphu udasoghano kuvechela mau la Mulungu. 45 Wayahudi yapoadaona msonghano adajazidwa ndi nchanje kuyenena mau yadachucha viudhu vidakambidwa ndi Paulo ndi kumtukwana. 46 Nampo Paulo ndi Barnaba adanena kwa mphamvu ndi kunena idali ndi ya kukulupalila kuti mau la Mulungu likambililidwe pakuyamba kwa anyiimwe pauti mulitaila kwa kutali kuchoka kwa anyiimwe ndi kujhiona kuti simafunikile umoyo opitilila penyani siti wang'anamukile ajhiko. 47 Ngati umo Atate atilamulila kunena nakuikani anyiimwe ngati dangalila kwa wandhu ajhiko kuti mpeleke chipulumuchi kwa madela yonche ya jhiko.'' 48 Mayiko yapo adavela ili adakondwa ndi kulemekeza maula atate ambili adasagulidwa kwa umoyo opitilila adakulupalile. 49 Mau la Atate lidainela jhiko lonche. 50 Nampho wayahudi adapempha yawoadajhichocha ndi wachikazi chamuhimu naponcho ndi ochogoza wa muijhi yaya yadasongozela mavuto kwa Paulo ndi Barnaba ndi kwataya kubwalo pa malile ya mujhi. 51 Nampho Paulo ndi Barnaba adakung'undha malifumbi ya myendo yawo pakutela adapita ku mujhi wa Ikonia. 52 Ndi opinzila adajhazidwa ndi chimwemwe pamojhi ndi mzimu oyela.

Chapter 14

1 Idachokela Kuikonio kuti Paulo ndi Barnaba adalowa pamoji mu sinagogi la Ayuda ndi kucheza mtundu umene gulu lalikulu la wanthu Ayuda ndi Ayunani adakulupilila. 2 Nampho Ayuda alije ulemu adasongozela njelu wanthu samanjiwe Mulungu ndi kuachita akale ipa kwa abale. 3 Kwa icho adakala kumene nyengo yaitali ndi acheza kwa mphavu ya Mulungu wamachita zokuza utenga wa chimwemwe chake wadachita chimwechi vodabwicha vichitike kwa manja ya Paulo ndi Barnaba. 4 Nampho malo yayakulu ya muji yadagawika wanthu akumoji adali pamoji ndi Ayuda ndia kumoji adali pamoji ndi otumidwa. 5 Nyengo osajiwa Mulungu ndi Ayuda amayesa kuakambila achogoleli wao kuachitila voipa ndi kuaponya myala Paulo ndi Barnaba. 6 Adajiwa limenelo ndi kutawila mu miji ya likaomia Listra ndi Derbe ndi malo yazungulila paja, 7 Ndi kumeneko adalika utenga. 8 Ndi Kulistra kudali munthu mmoji wadakala walije mphavu mmyendo mwake olumala chiyambile mmimba mwa amake siwadaendepo. 9 Munthuyu wadamvela Paulo ndi wakamba Paulo wadampnya molimbikila ndi kuona kutiwadali ndi chikulupi cho chilichidwa. 10 Kwa icho wadamkambila kwa mphavu imakwa myendo yako yuja munthu wadadumpha kumwamba ndi kuyamba kuenda. 11 Gulu yapo lidaona icho wachila Paulo adakazomoka mu mkambo wa kilikanio milingu yatichikila mu mtundu wa wanthu. 12 Adamtana Barnaba ''Zeu'' ndi Paulo ''Herme'' ndande wadali okamba wamkulu. 13 Wamkulu wa nchembe wa Zeu iye hekalu lake lidali kubwalo kwa muji wadapeleka mphango wa ng'ombe ndi mtungo wa madua mbaka pakomo pa muji iye ndi gulu la wanthu adafuna kuchocha nchembe. 14 Nampho otumidwa Barnaba ndi Paolo yapo adavela yaya adapwatula vovala vao ndi mwamsanga adapita kabwalo pagulu ndi adalila. 15 Ndi kukamba anyiimwe wanthu ndande chiyani muchita vinthu wi? Ife nafe wanthu tili ndi magani zo ngati yanu tikupelekelani utenga wabwino kutimng'amuke kuchoka kuvinthu vopande mate ndikumchota Mlungu walimoyo wadalenga kumwamba ndi fiko la ponchi ndi myanja ndi vilimkatimwake. 16 Nyengo yopita wadaavomeleza wanthu osachata Mlungu kuenda mnjila zao. 17 Nampho ikali siwadachoke popande mboni mmenemo wadachita bwino ndi wadaapacha mvula kuchoka kumwamba ndi nyenga yobalicha waapacha chakudya ndi chimwemwe mmitima mwao. 18 Pa mau yaya paolo ndi Barnaba kwa mavuto adaakaniza gulu kuachochela nchembe. 19 Nampho akumoji mwa Ayuda kuchoka Kuantiokia ndi Kuikonio adaja kukambila gulu adambula myala paoloo ndi kumkwekweta mbaka kubwalo kwa muji ndi amaganiza wafa. 20 Ingakale chimwecho opunzile adali pafupi ndi iye alimalima wadauka adalowa mmuji siku ya kawili wadapita kudebe ndi Barnaba. 21 Yapo adapoyaluza utenga wa Mulungu mmoji uja ndi kuachita opunzila ambili, adabwela Kulistra mbaka Kuikoniamu ndi mbaka Kuantiokia. 22 Adaendekela kulimbikila mizimu ya opunzila ndi mtima kuendekela muchikulupi, "wadakamba nditu tilowe mu ufumu wa Mulungu kupitila mavuto yambili." 23 Yapo adasankha waakulu akansa la okulpilila ndi atokuapemphela ndi kumanga osadya, adaaika mmanja mwa Ambuye iye anyiiwo amamkulupilila. 24 Ndipo adapia mu Pisidia, adafika ku Pamfilia, 25 Nyengo amacheza mau mu Perga, adachika kupita ku Atalia. 26 Kuchokela kumene adakwela sitima mbaka Kuantiokia kumene adali ajichocha, kwa lisungu la Mulungu kwa ndande ya nchito imene chapano adali aikwanilicha. 27 Yapo adafika Kuantiokia na Kuakusa wanthu pamojhi, nde adachocha nkhani ya vinthu vimene Mulungu waachitika ndi ntundu wadaachakulila chicheko cha chikulupi kwa wanthu a Maiko ina. 28 Adakala kwa nthawi ya itali ndi opunzila.

Chapter 15

1 Wanthu akuti adachika kuchokela Kuuyahudi ndi kuwayaluza achaabale adakamba ''ngati simuumbalidwa ngati dongosolo la Musa simukhoza kuomboledwa''. 2 Nyengo Paulo ndi Barnaba yapoadali ndi mpikisano ndi kukambilana pamojhi nao acha abale adalamule kuti Paulo Barnaba ndi wia apite Kuyelusalem kwa atumiki ndi okota kwa chifuko cha funcho ili. 3 Kwa chimwecho pakutumidwa kwao ndi kanisa adapitila Kufoinike ndi kusamaria kulengeza kunganamulindua maganizo. Adapeleka chisangalalo chachikulu kwa achaabale onche. 4 Yapo adajha Kuyerusalem adakhalbishidwa ndi kanisa ndi atumiki ndi azee ndi adazifikicha nkhani za vinthu vonche ivo Mulungu wavichita pamojhi nao. 5 Nampho wanthuakuti yao adavomela yaoadali pagulu la afalisyo adaima nd kukamba nimate kuwaumbala ndi kuwalamula aliguile thauko lamusa. 6 Chimwecho atumiki ndi azee adaima pamojhi kuiganizila ii nkhani. 7 Pamalo pakamba nyengo ya itali, Petro wadaima ndi kukamba kwa anyaiwo, "abale mujhiwa kuti nyengo ya bwino iyoyapita Mulungu wadachita lisankho pakati panu, kuti kwa mlomo wanga maiko yavele mau la ulaliki, ndi kuvomela." 8 Mulungu, uyo waijhiwa mitima, watilila umboni wa apacha mzimnu oela, ngati umo wadachitilakwathu. 9 Ndi siwadakonje kusiyana pakati pathu ndi anyaiwo, wadaichita mitima yao bwino. 10 Kwa chimwecho kwa chiyani mumuesela Mulungu kuti mwike nchinda pamwamba pa makosi ya opuzila yayo ata acha atate wanu ata ife sitikhoza kuembekeza? 11 Nampho tivomela kuti sitilamichidwe kwa mwawi wa Ambuye Yesu, ngati umo adali.'' 12 Msonkhano onche udakhala chete yapoamamvechela Barnaba ndi Paulo yapo amaichocha nkhani ya langizo ndi vozizwicha ivo Mulungu wadavichita pamojhi ndi anyaiwo pakati npa wanthu amaiko. 13 Yapo adasiya kukamba yakobo wadayankha ndi kukamba abele nivecheleni. 14 Simoni wakambilila payamba mulungu kwa mwawi wadaathangatila maiko kuti wajhipatile kuchoka kwao wanthu kwa chifuko cha jhina lake. 15 Mau ya olosa yadavomelezana ndi ili ngati umo lidalembedwela. 16 Pamulo pa vinthu ivi sinibwele ndi kuimangancho hema ya Daudi iyoidagwa panchi sindiikweze ndi kuibweezela uzene wake. 17 Kuti wanthu anyiyao akhalila amfunufune ambuye pamojhi ndi wanthu amaiko yao atanidwa kwa jhinalanga. 18 Umu ndeumo wakambila ambuye uyo wachita vinthu ivi vijhiwikana kuyambila nyengo za kale. 19 Chimwecho basi ganizo alanga ni kuti sitidaapacha vuto wanthu amaiko amng'anamukila mulungu. 20 Nampho tilembe kwao kuti ajhipatule patali ndi kuwanangika kwa chifani kumbilo la uhule ndi ivovamangidwa ndi mwazi. 21 Kuchokela abanzi wa okota kuli wanthu pakati pa kila mujhi olalikila ndi kumsoma Musa pakati pa masinagogi kila sabato.'' 22 Kwachimwecho idaonekana kuti idaakwadilicha atumiki ndi okota pamojhi ndi kanisa lonche kumsankhula Yuda uyuwadatanidwa Barsaba ndi silas adali ochogaza kanisa ndi kwaatuma kuantiokia pamojhi ndi Paulo Barnaba. 23 Alemba chimwe atumiki okota ndi abale kwa abale amaiko anyiyaodali kuantiokia kushamu ndi kukilikia salamu. 24 Tidavela kuti wanthu akuti yaositidaapache lamulo limenelo adachoka kwathu ndi wadavuticha kwa mayaluza yapeleka vuto mmitima mwanu. 25 Kwaicho yaonekana bwino kwathu taonche kusankula wanthu akwatuma kwanu pamojhi ndi okondedwa wanthu Barnaba ndi Paulo. 26 Wanthu yao adakhaikicha umoyowao kwa chifuko cha jhina la Ambuye Yesu Kristo. 27 Kwa chimwecho tamtuma yuda ndi sila saakukambileni vinthu vimenevo vonche. 28 Pakati yaonekana bwino kwa mzimu oela ndi kwathu usaika pakati panu katundu wa ukulu kupitilila yaya yali ya lamulo. 29 Kuti mng'anamuke kuchoka kuvinthu vichoka kwa chifani mwazi vinthu va kuphedwa ndi uhule ngati simujhiike kwa kutali ndi vinthu ivi siikale bwino kwanu zikomu.'' 30 Chimwecho basi umodamwazidwila adachikila kuantiokia pamalo posonkhanicha msonkhano pamojhi adafikicha kalata. 31 Yapo adaisoma adasangala kwa chifuko cha kwaathila mtima. 32 Yuda ndi sila ndi olosa wadaathila mtima abale kwa mau yambili ya kaathila mphavu. 33 pamolo pakukhala nyengo yakuti kumeneko umoanda mwaziduiila kwa mtendele kuchokela kwa abale yaoadatumidwa. 34 nampho iaonekana bwaino sila kukukhala kumweke . 35 nampha paulo ndi wina yao adakhala kuaantiokia pamojhi ndi wiina ambilinyiyala adayaluza ndi kulalikila maula ambuye. 36 pambuyo pa siku za kuti paulo wadakamba kwa baranaba ndi tijhibuala chapano ndikwaendela achabale pakati pakila mujhi yapo talalikila mau la ambuye kwa kwaona umo ali. 37 barnaba wadafuna kumtenga pamojhi nao yahana uyowadatanidwa marko. 38 nampho paulo wadaganizila sati buino kumtenga marko uyowadaasia kumeneko kupamfilia ndikela nao kunchito . 39 pothela padachokela kuchuchana kwa kukulu kwa chimweko adapatulana ndi arnaba wadamtenga morko ndi kunyamuka kwa. sitima mbaka kukipro. 40 nampho paulo wadamsankhula sila ndi kuchoka pamalo popachidwa ndiachabale pakati pa mwawi wa amuye . 41 ndi wadapita kupitila kushamu niwamicha mkanisa.

Chapter 16

1 Paulo nae yaphowadajha derbendilystra ndi phenya adalipho ndi ophuzila wathanidwa Timotheo ni mnyamantha uyowadabadwa ndi mamawakiyahudi ambayo ni muumini ndi baba wake mgiriki. 2 Wantu wa listra ndi ikonia adamuhakikisha bwino. 3 Paulo wadamfuna ili wasafilinae chimwecho adamuthenga ndi kumnthalili kwa chifuko chawayaudi anyiyaoadaliko kumeneko kwani oucheadamjhiwa kuti baba wake nimgiriki. 4 Yapoadali amaphiutha adaphitila kumaiko kumaiko ndikuchocha maagizo kwa makanisa ili kuyatii maagizo yaya yadalembedwa ndi mitume ndi azee huko kuyerusalemu. 5 Chimwecho makanisa yamaimarishidwa katika imani ndi anyiyao adaamini adaongezeka kwa idadi ya kilasiku. 6 Paulo ndi achanjake adaphita Filigia ndi Galatia kwani Roho wa Mulungu wadakhaniza kuhubiri mau kumeko kujimbo la Asia. 7 Yapo adakhalibia kimisia ada Yesu kuphintha Bithiania nampho roho wa Yesu wadakhaniza. 8 Kwa chimwecho adaphita kumisia adaja mpaka kijiko Troa. 9 Maono yadamchokela paulo makedonia. 10 Paulo yaphowadaona maono mara adajhiandaakuphita makedonia ndiwajhwa kuti mulungu waanthitana kuphintha kuwahubilia injili. 11 Chimwecho nthidachoka kuchoka troa adaphita moja kwa moja kwa moja samothrake ndi siku iyodachata adafika kujikolaneopali. 12 Kuchoka pamenenthidaphita filipi ambaphonimoja ya majhiko ya makedonia jhiko muhimuu kupitila wilaya ndi utawala wakinimi ndi tidakhala siku kadhaa. 13 Siku ya sabato tidaphita kubwalo kwa chicheko kwa njila ya mchinje sehemu ambapo thidaganizila sikukhale pamalo pochitila maphephelo tidakala phanchi ndi ndikukamba ndi anyazimai anyiyaoadaja pamoji. 14 Wamkhazi mmoji watanidwa lidia ugulicha mazambarau kuchokela katika muji wa tiatira mwene wamamuyamika mulungu wadativechelo ambuye adamchakula mtima wake ndikuika maanani mau yadakambidwa ndi Paulo. 15 Pambuyo pakubatiza iye ndi nyumba yake yonche adathondoza wadakamba ''ngati mwaniona kutiine ni oaminika kupitila ambuye basi ndikuthozani mulowe ndi khukala kwanga'' wadathuthoza kwabasi. 16 Ikakala kuti yapotidali timaphita phamalo pa maphemphelo wamkazi mmoji uyowadali ndi pepo la utambuzi wadapezana nafe wadampelekela ambuye wake faida ya mbili kwa kubuni. 17 Wamkazi uyu wadamchata Paulo pamoji ndi ife ndi watimbakelele ndi kukamba ''anyiyawa wachimunaniatumikiwa mulungu wali wamkulu anyiyao watangazila anyiimwe ukhani ya uokovu. 18 Wadachita chimwecho kwa siku za mbili nampho wa kakhala waiphichidwa ndi vichoto chimecho wadanganamuka kumbuyo ndi kumkambila pepo ''nikulamu la kwa jina la Yesu umchoke mkati mwake'' naye wadachoka ndi kumsia mara kamoji. 19 Achaambuye wake yapoadaonakuti tumanila faida yao lachoka adagwila Paulo ndi sila ndi kwakweketa kusokoni mbale ya achinawene olamula. 20 Yapoadafikacha kwa mahakimu adakamba ''anyiyawa wachimuna ni wayahudi ndi achiticha fujho ya ikulu kupitila mujhi wanthu. 21 Ayaluza vinthu ambavo osati sheria ife kuyala ndilo walakuyachta ngati warumi.'' 22 Guru lidang'anamukila kumbuyo Paulo ndi Sila, mahakimu mahakimu adang'amba nchalu zao ndi kwa vula ndi kwaramula atyapidwe viboko. 23 Pambuyo pakuwatyapa viboko vambili adatayakugereza ndi kwaramula askari wa gereza kuwalinda bwino. 24 Pambuyo polandila maramulo yaya, askari agereza adataya katika chumba cha mkati mwa gereza ndikwamanga myendo yao. 25 Nyengo ya usiku wa manane, Paulo ndi Sila adali amaphempha ndi kuimba nyimbo za kumtuza Mulungu, uku wafungwa wina amavechela. 26 Gafra lidachokela tetemeko lalikulu ndi misingi ya gereza idatingizidwa, vicheko va gereza vidachakluuka ndi minyororo ya afungwa yonche idalegea. 27 Mlonda wa gereza wadauka kuchokela kulitulo ndi waona vicheko vonche vagereza vachakulidwa; kwachimwecho watenga upanga wake chifuko wamafuna kujiwa kwa ndande wadaganiza omangidwa onche adathothawa. 28 Nampho, Paulo wadatimba kelele kwa sauti ya ikulu wadakamba, "siudajipweteka kwa ndande thaonche tili pamalo pano." 29 Mlonda wa gereza wadaphempha taa zipelekedwe ndi wadalowa mkati mwa gereza kwa chisangu, ndi watentemela ndi kuopa, wadagwela Paulo ndi Sila. 30 Ndi kwachocha kubwalo kwa gereza ndi kukamba, "olemekezedwa, nichite chiyani chiyani ili nipate kuokoka?" 31 Nao adamkambila, "mwamini Ambuye Yesu nawe siuokoke pamoji ndi nyumba yako." 32 Adakamba mau la Ambuye kwake, pamoji ndi wanthu wonche kukomo kwake, 33 Mlonda wa gereza wadatenga usiku uuja ndi kwasambiza sehemu izoadapwetrekedwa, iye pamoji ndi wantu akukomo kwake adabatizidwa kamoji. 34 Wadapeleka Paulo ndi Sila kukomo kwake ndi kuwapilila chakudya. Nae wadali ndi chisangalalo chachikulu pamoji ndi akukomo kwake kwa chifuko adamwamini Mulungu. 35 Yapo idali usana, mahakimu adapenkhani kwayujha mlonda wa gereza adakamba, "Alamuleni anyiwajha wantu ajipita." 36 Mlonda wa gereza wadamjiwicha Paulo pakati pamalo yaja yakuti, "mahakimu apekankhani nilamule muchoke; kwachimwecho machokani kubwalo ndi mjipita kwa mtendele." 37 Napho Paulo wadakambila, "adatimenya pahadharani wanthu ambao ni Warumi bila kutihukumu ndi adalamula kutitaya kugereza alafu chipano afuna kutichocha kwasi? Palibe siigozeka, nao achinawene aje kutichocha pamalo pano." 38 Alonda adajiwicha mahakimu pakati pamau yaya mahakimu adaopa sana paja adajiwakuti Paulo ndi Sila ni Warumi. 39 Mahakimu adaja ndi kwatondoza achoke ndi yapo adachocha kubwalo kwa gereza, wadaphempha Paulo ndi Sila achoke kubwalo kwa muji wao. 40 Kwachimwecho Paulo ndi Sila adachoka kubwalo kwa gereza adapita kukomo kwa Lidia. Paulo ndi Sila yapoadaona abale, adatila moyo ndi potela kuchoka katika muji umeneo.

Chapter 17

1 Ni yapo adapita miji ya Amfipoli n Apolonia, adafika hadi muji wa Thesaonike ambao udali ni sinagogi la Wayahudi. 2 Ngati umoili kawaida ya Paulo, wadapita kwao, ni kwa muda wa siku zitatu za sabato wadakambana nao juu ya malembo. 3 Wadali kwavunukulila malembo ni kwaelekezo kuti idambidi Mpulumusi wazunjidwa ni pambuyo kuhyuka nchho kuchoka kwa akufa. Wadakambila, uyu Mpulumusi nikukambilani nkhani zake ndo olamicha. 4 Baazi ya wayahudi adavomela ni kuungana ni Paulo ni Sila, pamoji ni Wagiliki akumjiwa Mulngu, anyamame ambili adang'anamuka ni kundi la likulu la wanthu. 5 Nampho akumoji Wayahudi adakulupalila anyiyao ajala nchanje, adapita kumsika ni kwatenga baazi ya wanthu oipa, adakusanya gulu la wanthu pamoji, nikusababisha vulugu kumjini, baadae adaivamia nyumba ya Jasoni ni afuna kwagwila Paulo ni Sila dala kwapeleka pachogolo pawanthu. 6 Nampho yapo wadakosa, adamgwila Yasoni ni baazi ya chabale wina ni kwapeleka pachogolo pa maofisa amuji, abula pokoso "anyiywa wachimuna aling'anamula jiko afika mpaka kunoncho." 7 Wachimuna anyiyawa akaribishidwa ni Yasoni awananga lamulo la Kaisari, akamba kuli mfumu mwina watanidwa Mpulumusi.'' 8 Unyinji wa maofisa amuji yapo adavela vichito vimenevo, adajalidwa ni kuopa. 9 Baada ya kuti atokala atenga ndalama ya mbili ya kulindila kuchokakwa Yasoni ni wina, wadasia apite. 10 Usiku uja achabale adamtuma Paulo ni Sila Beroya. Ni yapo adafika kuja adapita katika sinagogi la Wayahudi. 11 Wanthu anyiwaja adali ali ni kuelewa kwa mbili kuliko anyiwaja wanthu Akuthesalonike kwa ndande adali ajiandaa kulilandila mau kwa njelu zao, ni kuzuzumila malembo kila siku dala kuona ngati mau yanenedwa yali chimwecho. 12 Kwa icho ambili wao akulupalila, akakalamo wachiazi ali ni uwezo waukulu wa Kigiriki ni wachimuna ambili. 13 Nampho Wayahudi ni Wathesalonike adagundua akuti Paulo watangaza mau la Mulungu Kuberoya, adapita kumeneko ni kukwinjizila ni pamwepo kuyambicha ndeo kwa wanthu. 14 Kwa nisanga, achabale ampeleka Paulo kwa njila ya nyanja, nampho Sila ni Timotheo adakala pampaja. 15 Anyiwaja achabale adampeleka Paulo adapita nae mpaka Kuathene. Yapo adamsii Paulo kumeneko, adalandila malangizo kuchoka kwake kuti, Sila ni Timotheo aje kwa iye kwa chisanga umo ikozekanila. 16 Ni nthawi niwalindilila kumene Kuathene, mtima wake udadandaulichidwa mkati mwake kwa umo wadaonela muji umo wati kujala. 17 Chimwecho adakambilani katika nyumba ya Mapemphelo ni Wayahudi anyiwaja amjiwa Mulungu ni kwa anyiwaja onche wazana nao kila siku kumsika. 18 Baazi ya wanafalsafa Awaepikuleo ni Wastoiko adamsendelela. Ni wina adakamba, "ni chiani icho wachikamba uyu mkambaji wamng'ono?" Wina akamba, "ionekana walalikila nkhani ya Mulungu mlendo," Kwandande walalikila nkhani ya Mpulusi ni kuhyushidwa. 19 Adamtenga Paulo nikumpeleka Areopago, amakamba, "tikoza kujiwa yaya mayaluzo yampya yayo uyakamba?" 20 Kwa ndande upeleka vichito va mpya katika makutu yatu. Kwa icho tifuna kujiwa yaya mambo yali ni mate yanji?" 21 (Ni wanthu onche Akuathene pamoji ni alendo alipo kwao, atumia muda wao ata katika kukamba ni kuvechela juu ya jambo lampya.) 22 Kwa icho Paulo wadaima pakatipakati pa wanthu Areopago ni kukamba, "Anyiimwe wanthu Akuathene, nione kuti anyiimwe ni wanthu adini kwa kila ntundu, 23 Kwani katika kupita mwanga ni kupenyelela vinthu vanu va mapemphelo, napenya mau yalembedwa kumadhabahu yanu yakamba, "KWA MULUNGU WAJUWIKANA." Chimwecho basi uyo mumphemphe bila kujiwa, ndiiye nikujuwishani anyiimwe. 24 Mulungu uyo wakonja jiko, ni kila kanthu chili mkati, pakuti ni Ambuye akumwamba nipanchi, siakoza kukala katika nyumba nyumba zakonjedwa kwa manja. 25 Ni pia siwatumikilidwa ni manja ya wanthu kuti wafuna chinthu kwa nyiio, kwani iye mwene wapacha wanthu umoyo ni pumzi ni vinthu vina vonche. 26 Kupitila munthu mmojhi, wadaita maiko yonche ya wanthu akala pamwamba pa mphumi ya jhiko ni wadaikila nthawi ni malile katika malo akala. 27 Kwa icho afunika kumfunafuna Mulungu, ni yapasa amfikile ni kumpata, ni kwa uhakika siwali patali ni kila mmoji watu. 28 Kwa iye tikala, tienda ni kukala ni umoyo watu, ngati uja otunga wanu mmoji wanu wa shairi yapo wadakamba, "tiliobadwa wake." 29 Kwa icho ikakala, ikakala ife ni obadwa a Mulungu, siifunika kuganizila kuti Uungu ni ngati dhahabu, au shaba, au myala, chosepedwa chasepedwa kwa ubwino ni maganizo ya wanthu. 30 Kwa icho, Mulungu wadakalila chete nyakati zijaza kuwewela, nampho saino walamua wa nthu onche kila pamalo apate kupempha. 31 Ili kwa ndande waika siku iyo siwalamule jiko kwa zene kwa munthu uyo wadamsankha. Mulungu wadachocha uhakika wa munthu uyu kwa kila munthu paja wadamhyusha kuchoka kwa akufa. 32 Ni wanthu Akuathene yapo adavela nkhani ya kuhyushidwa akufa, wina wao adamtukana Paulo, ila wina adakamba, "tikuvechelancho kwa nkhani ii" 33 Pambuyo pake, Paulo wadasia. 34 Nampho baazi ya wanthu aungana nae adakulupalila, wakakalamo Dionisio, ni wamkazi watanidwa Damari ni wina pamoji nao.

Chapter 18

1 Baada ya vinthu vimenevo, Paaulo wadachoka kupita Kukorintho. 2 Kumeneko wadampata Myahudi watanidwa Akwila munthu wa kabila la Ponto, iye ndi mkazake watanidwa Prisila adaja kuchoka kumeneko Kuitalia, kwa chifukwa Klaudia wadalamula Wayahudi onche achake kurama, Paulo wadaja kwao; 3 Paulo waishi ndi kuchita nchito nao kwani iye wachita nchito ilingana ndi anyiiwo anyiiwo adali ndi akonja mabanda. 4 Paulo wadapatakaz nao mkati mwa nyumba mwa mapemphelo kila siku ya sabato. Wadaanyengezela Wayahudi pamoji ndi Wagiriki. 5 Nampho Sila ndi Timotheo yapoadaja kuchoka Kumakedonia, Paulo wadasukumidwa ndi mzimu kwaalangiza Wayahudi kuti Yesu nde Kristo. 6 Nyengo Wayahudi amamkanila ndi kumpepula, mchimwecho Paulo wadakung'untha nchalu zake pachogolo pao, ndi kwaambila, "mwazi wanu ndi ukale pamwamba pa myutu yanu mwachinawene, ine ndilibe kosa. Kuchoka saino ndi kuendekela, ndachata apajiko." 7 Mchimwecho wadachoka paja wadapita kunyumba ya Tito Yusto, munthu uyowamgwadila Mulungu. Nyumba yake ili karibu ni nyumba ya mapemphelo. 8 Krispo, wamkulu wa nyumba ya mapemphelo pamojindi wanthu amnyumba mwake adamkulupalila Mbuye. Wanthu ambili wa Korintho yapoadamvela Paulo ndi wakamba adaklupalila ndi kubatiza. 9 Ambuye adamkambila Paulo usiku kwa njila ya maroso, "usidaapo, nampho kamba ndi usidakala kachete. 10 Kwani ine ndi pamoji nawe, ndi palibe uyasiwaese kukuchita choipa, pakuti ndili ndi wanthu ambili mkati mwa muji uu." 11 Paulo wadakala kumeneko kwa muda wachaka chimaji ndi myeezi sita ndi wayaruza mau la Mulungu mkati mwao. 12 Nampho Galio yapo wadachitidwa kukala olamula wa Akaya, WAyahudi adaima pamoji asagwilizane ndi Paulo ndi kumpeleka pachogolo pa mpando wa lamulo. 13 Adakamba, "munthu uyu wanyengezela wanthu amgwadile Mulungu kumbuyo ndi ramulo." 14 Nyengo Paulo yapo wamafuna kukamba, Galio wadaakabila Wayahudi, "anyiimwe yahudi, ngati idakankala kasa au kuwananga, idakakala uzene kuwapotela nchito. 15 Nampho kwa chifuwa ndi mafunchidwe, yayo yahusu mau ndi majina, ndi lamulo la, Basi lamujlani anyaimwe mwachinawene sindikumbila kukala olamula kwa makambidwe ya vichito vimenevo." 16 Galio wadalamula achoke pachogolo pa mpando wa lamulo, 17 Mchimwecho, adamgwila Sosthene, wamkulu wa nyumba ya mapemphelo, adambula pachogolo pa mpando wa lamulo. Nampho Galio siwadaganizila icho adachichita. 18 Paulo, baada ya kukala paja kwa nthawi ya Itali, wadaasia achaabale ndi kupita kwa chombo siria pamojin ndi Prisila ndi Akwila kabla ya kuchoka padooka, wadameta chichi lake lonche kwani wadalapa kuti osunga lamola. 19 Yapo adafika Kuefeso, Paulo wadamsia Prisila ndi Akwila paja, nampho iye mwene wadalowa mnyumba ya mapemphelo kufotokozelana ndi Wayahudi. 20 Yapo adamkambila Paulo wakale nao kwa nyengo ya yitari, iye wadakana. 21 Nampho wadachoka kwao, wadaakambila, "sindibwelencho kwanu, ikakala ndi kwa chikondi cha Mulungu." Baada ya pamenepo, wadacheka kwa chombo kuchoka Kuefeso. 22 Paulo yapatula Kukaisaria, wadakwela kupita Kusamaria kunyumba ya mapemphelo ya Kuyerusalemu, ndeyapo wadachika panchi kwa anyumba ya mapemphelo ya Antiokia. 23 Baada ya kukala kwa nthawi paja, Paulo wadachoka kupita kumalo kwa Galatia ni Frigia ndi Kwaatila mtima opuzila onche. 24 Myahudi mmoji watanidwa Apolo, uyowadabadwa kumeneka ku Alexandria, wadaja Kuefeso wadali ndi uzene mkati mwa kukamba ndi bidii mkati mwa malembedwe. 25 Apoli wadaelekezedwa pakati pakuyaruza kwa Ambuye kwa chifukwa umowadali ndi bidii mkati mwa mzimu, wadakamba ndi kuyaluza kwa uzene vichito vimuhusu Yesu, nampho wadaujiwape ubatizo wa Yohana. 26 Apolo wadayamba kukamba kwa mphavu mkati mwa nyuma ya mapemphelo. Nampho Prisila ndi Akwila yapoadamvela, adachita ubwenji naye ndi wadaelezea pamwamba pa njila ya Mulungu kwa uzene. 27 Yapo wadakhumbila kuchoka kupita kwa Akaya, achaabale adamtila mtima ndi kwalembela karata opuzila anyiyawo ali ku Akaya ili apate kumlandila. Yapo wadafika kwa neema wadatangatila sana anyiwaja adakhulupalila. 28 Kwa mphavu zake ndi njeru, Apolo wadaazidi Wayahudi pawazi ndi walangiza kupitila malembedwe ya kuti Yesu nde Kristo.

Chapter 19

1 Idali Apoolo yapowadali ku Korintho, ndi Paulo wadaendela maiko ya pamtuna ndi kufika pa mujiwa Kuefeso, ndi wadaasumana omphumira akuti kumeneko. 2 Paulo wadaakambila, bwanji mudalandila mzimu oyera yapo mudakulupalila?'' Adamkambila, noto, sitinakhoze kuvelapo za mzimu oyera.'' 3 Paulo wadakamba chipano anyiimwe mudabatizidwa bwanji? Adakamba tidabatizidwa ndi Yohana. 4 Nampho Paulo wadayankha, "Yohana wadaabatiza ubatizo wakulapa, wadaakambila anyiwajha wnthu kuti afunika kumkhulupilila yujha iye wakadajha pambuyo pake kuti ndi Yesu." 5 Munthu yapoavela nkhani iyi adabatizidwa mjhina la Yesu. 6 Ndiidali kuti Paulo yapo wasanja manja, Mzimu Oyera wadachikila ndi adaba kukamba pa mikambo yolekanalekana ndi kulalika mau ochokela kwa Mlungu. 7 Pamoji adali wachimuna khumi ndi awili. 8 Paulo wadalowa mnyumba ya maemphelo ndi kuyamba kukamba wadakhala pa myezi itatu. wamakhambana ndi wanthu ndi kwaguza wanthu pa nkhani ya ufumu wa Mulungu. 9 Nampho Ayahudi wina adali ouma mitima ndi osafuna kukhulupilila, adayamba kukhamba mau yoipa pakati pa njila ya Kristo pamaso pa gulu. Nampho Paulo wadasiyana nao ndi kuwasankha okhulupilila patali ndi anyiio wadayamba kukamba masiku yonche mnyumba ya Tirano. 10 Izi zidaendekela pa zaka ziwili anyiyao amakha Kuasia adavela mau la Ambuye, onche Ayahudi ndi Ayunani. 11 Mulungu wamachita vichito vavikulu kujela manja ya Paulo. 12 Kuti ingakale odwala adalamichidwa, ndi mizimu yoipa idaachoka, yapo adatenga chitambaya ndi nchalu zochoka mthupi la Paulo. 13 Nampho padali ndi Ayahudi ochocha mizimu yoipa adaenda enda kujela malo yaja adatumikila jhina la Yesu pa ndande zao achinawene ndi kuakambila anyiwaja adali di mizimu yoipa, kukamba ndikulamulani muchoke pa jhia la Yesu uyo Paulo wamlalikila. 14 Adazichita izi adali wana asano ndi awili wa ankulu wa nchembe Wachiyahudi, Skewa. 15 Mizimu yoipa idayankha, Yesu ndi mzindikila ndi Paulo ndi mzindikila nampho anyaimwe achiyani? 16 Ujha mzimu oipa mkati mwa munthu udalumphila ochocha mizimu yoipa ndi kuwamenya ndeyapo adathawa kuchoka mnyumba muja ali maliseche ndi apwetekedwa. 17 Izi zidajikana ndi wonche, Ayahudi ndi Ayunani, yawo amakha kumeneko ku Efeso ndi adali ndi mantha kupunda, ndi jhina la Ambuye lidapambana kulemekezeka. 18 Akristo ambili adaja ndi kulapa ndi kulangiza vichito vao voipa ivo adachita. 19 Ambili amachita ung'anga udasonkhanicha vikalakala vao, ndi kubucha moto pa maso pa waliyonche, nyengo anyaio adawelenga mtengo wa vinthu vija, idali vibanthu makumi asano. 20 Kwaicho mau la Ambuye lidakula kupunda. 21 Paulo kukwanicha nchito yake kuja ku Efeso Mzimu udamchogoza kupita ku Yerusalemu kujela ku Makedonia ndi ku Akaya; wadakamba pambuyo pokala kua, ndifunika kupita ndi ku Rumi. 22 Paulo wadatumiza omphunzira ake awili kupita ku Makedonia. Timotheo ndi Erasto yao amamthandiza. Nampho mwene wake waakhala ku Asia pa kanthawi. 23 Nyengo imeneyo padachokela chipolowe cha chikulu ku Efeso pakati pa njila ija. 24 Wanchito za siliva mmojhi jhina lake Demetrio, wadakonja timafanizo la ndalama ya mulungu Diana wadapeleka malonda yayakulu kwa anchito wake. 25 Kwaicho wadasonkhanicha anchito ija ndi kukhamba, olemekezeka mjiwa kuti pa malonda yaya ife tipheza makobili ya mbili. 26 Muona ndi kuwela kuti, osati pano Paefeope, nampho pafupi Asia yonche, uyu Paulo waaguza wanthu ambili ndi kuang'anamula wakamba kuti palije milungu iyo yachitika ndi manja. 27 Ndi osatipe malonda yathu yalimmavuto, siyakhale siyafunikancho, nampho nyumba ya Mulungu wamkazi wali wamkulu Diana siwaoneke walije mate, ndi wakhoza kuluza ukulu wake iye Asiya ndi jhiko amphemphera.'' 28 Yapo adavela izi adajalidwa ndi mphwayi ndi kuchita mapokoso ndi kukamba kuti Diana wa Kuefeso ndi wamkulu. 29 Muji wonche udajala chisokanizo, ndi wanthu adatawa pamoji mbwalo la masewela adagwilidwaoyenda njila anjake ndi Paulo, Gayo ndi Aristarko amechokela Kumakedonia. 30 Paulo wamafuna kulowa mgulu la wanthu na mpho omphuziza adamchekeleza. 31 Akulu aboma la Asia akumoji adali mabwenji lake adampelekela utenga wamphamvu kumuphempha wasadalowa mbwalo la masowela. 32 Wanthu akumoji amakamba ichi wina chija, ndande gulu la wanthu lidali lsokanizika, ambili samajiwe ndande chiyani adali pamoji. 33 Ayahudi adamtulucha Iskanda kubwalo kwa gulu la wanthu ndi kumkweza pamwamba pa maso pa wanthu. 34 Nampho yapoadajiwa kuti iye ndi Muyahudi wonche adachita mapokoso pa mau limoji pa nthawi, "Diana ndi wamkulu wa Kuefeso." 35 Pambuyo pa mlumbi wa mujiwo kuakalicha wanthu chhete, wadakamba, "anyiimwe waachimuna Akuefeso yani siwajiwa kuti muji uno wa Efeso ndi wasunga nyumba ya Diana wamkulu ndi ija piicha idagwa kuchokela kumwamba?" 36 Pakuona kuti izi sizikhozekana, tifunika kukhala chete ndi msachita chilichonche msanga. 37 Mate yake mwatana wanthu anyiyawa wakuakulu anchembe osati ankhungu a nyumbna ya Mulungu ndi osati onyoza Mulungu wathu wamkazi. 38 Kwaicho ngati Demetrio ndi anchito ali pamoji ndi iye ali ndi milandu pakati pa munthu waliyonche, bwalo la milandu lilipadanga ndi olamula alipo apelekedwe. 39 Ngati iwe ufuna chilichonche pa vinthu vinjake zikaveka ku msonkhano. 40 Uzene kuti tili pipa pakuimbicha mlandu pakusokaniza siku la lelo, palije ndande vuto ili ndi sitikoza kujikambilla. 41 Wakhate kukhamba yaya wadaakamba wanthu ajipita.

Chapter 20

1 Pambuyo potha phokoso, Paulo adatanisa ophunzila waja, nawalimbitcha mtima. Ndipo adawalaila iwo adachoka napata ku Makedonia. 2 Adayendela madela akumeneko, nalimbisa mtima wanthu ndi mau ambili pambuyo adapita ku Grisi. 3 Anakakhalako miyezi yitatu, pamene adali pafupi kupita ku Silia pachombo Ayuda anachita chiwembu. Pamenepo adaganiza zopita njira ya ku Makedonia. 4 Adampelekeza Sopatre mwana wa Piro, w ku Berea; Aristarko ndi Sekondo a ku Tesalonika, Gayo wa ku Deribe; Timotheo ndi Tikiko ndi Trofimo a ku Asia. 5 Koma wanthu adatha kusogela ndi adali akulindilila huja Tirowa. 6 Kwa panjila ya panyanja kufikila ku Filipi, pambuyo pa masiku amikae yapande choupisa ndi masiku asano tidafikila kuja ku Tiroa. Tidakala kumeneko masiku saba. 7 Pa siku loyamba la sabato, tidasonhana kuti tidye mgonelo, Paulo adakamba ndi anthu pakuti ankayembeza kupita umawa wake, adapitariza kukambawo mpekana pakati pa usiku. 8 Panali nyali zambil mchipinda cha golofa umo tidasonkana. 9 Pawindo panali mnyamatawina zina lake Utiko amene adalema ndi liturolamphanivu. Ata Paulo pamene amahubili amunthawi yaitari, nnyamata uyu adali atagona, adagwa pasi, kuchakela kumwamba kwa golofa aje katatu ndi adatondoledwa atefakale. 10 Kona Paulo adasika pasi naziponya pamnyamatayo namkhuambatrira, "ndi musanivutike pakuti ali moyo." 11 Ndipo adakwela kugholofa ndi anamenya mkate adadya. Pambuyo poamba ndi kwo mzithawa yayotari, mpakana umawa adanyamaka. 12 Ndipo anthu wajaadamutenga mnyamata uja wali wamoyo ndi montche akondwela kupunda. 13 Ife tidasogolela kukakwela chombo kupita ku Aso kumene tidaganizila kukamtengeka Paulo, iyeadakoza chimwechi chifukwa adafuna kupita pamtunda. 14 Pamene adafika ku Aso, lidamweza mzisitima tiapita ku mutulene. 15 Pambuyo pake ife tidachoka kumeneko ndi siku la kawili lidafika mbali ya ya kawiri ya chilumba cha Kio. Siku losatira tidafika chilumba cha samo ndi umawa wake lidafika muji wa Mileto. 16 Paulo dasimikiza zolambalala Efeso, kuopa kutaya nthawi kujiko la Asia; aankatulumila kuti ngati kotheka akathole ali ku Yerusalemu pa siku la Pentekosite. 17 Kuchoka ku Muleto adaluma wanthu mpaka Efeso ndi kwatana akulu ampingo. 18 Pamene adafika kwa iye adawakambila imwe mwawene mujiwa kuyambila siku yoyamba nidaponda pano pa Asia mmene nidali kwanu nthawi yonche. 19 Nkamtumikila Ambuye anozichepecha kupunda pakati pa zowawa ndi zomvuta zimene zidandogwela chifukwa cha viwembu va Ayuda. 20 Mujiwa kuti sindinakubisileni kanthu kalikonse koti nkuthandizen. Ndidakuhubilani nde kukuyeluzani poyela ndi mzinyumba zanu. 21 Ayuda ndi Agriki omwe ndidapempha kolimba kuti atembenukile kwa Mulungu molapa ndi kumakhuupilila Ambuye wathu Yesu. 22 Ndi sophano penyentehani ine ndikunivemeleza Mzimu Oyela kupita ku Yerusalemu, amene sindimaziwa zimene zikachitela ine kumeneko. 23 Kama pakuti Mzimu woyela akundichitila umboni ine, kuti mudzi uliontche akukamba kuti zowana ndi zopwetika ndizomene zikundidikila. 24 Hama sindiganiza zamayo wanga, ngati ndi wamitengo wapatari kwa ine, malinga ndikamaliza nchito yanga ndi utumiki uwo Ambuye Yesu adandipasa, kuti kulalika poyela uthenga wabwino mena za kukoma mitima kwa Mulungu. 25 Tchapano ndijiwa kuti ununu nzonche amene ndidaklalikilani za ufumu wa Mulungu, semuzaonaso nkhope yanga ai. 26 Chifukwa chake ndikuuzani monenesa lero, kuti ngati ena mwa inu atayike, izo nzake, une ndi libe mlandu. 27 Pajatu sindidakubisileni kanthu ai koma ndiolakulalikilani vontche vamene Mulungu afuna. 28 Mzimu Woyela adakuikani kuti mzipenyelela kanisa lyonche, nchipano mzisande mwene, ndi kusandaso kanisa. Wetani nkhos za kanisa la Ambuye, uo adaombola ndi mwazi wao. 29 Ndijiwa kuti ndakazachoka ine, pazalowa momblu yowopya pakati panu, iyo sizaelekelela nkhasazo. 30 Ngakhale pakati panu pomwe pazauka ena okamba vamtila ndi kumnyanga ophunzila kuti awasate. 31 Imwe khalani maso, kumbukilani kuti pa zaka zitatu ubana ndi usiku sindidaleke kukuyeluzani aliyenche mwa inu ndi misozi. 32 Mchiwechi sopano ndikukuikani mmanja mwa Mulungu, azaze yake woonesa kukoma mtima wake akusungeni bwino. Mauo ali ndi mphamvu za kukulisa mpingo, ndi kukupeni madaliso yontche yayo Mulungu akusungulani wanthu wake. 33 Sindakolakhumbile ndarama kapena zomvala za munthu aliyetche ai. 34 Imwe mjiwa kuti manja angawe adagwila nchito kuti ndipeze vinthu vimene ine ndi azangavematisowa. 35 Pa vontche ndakupatchani kuti pakugwila nchito kolimba, chimwechi olimba, tiyenela kuthandiza oofoka. Kumbukilani mau a Ambuye Yesu akati kupesa koposa kulandila. 36 Yapo Yesu adakamba vimenevi adagwada pesi namphepete nawo pamoji ena wotche waja. 37 Wontche adalire kupunda. Adamkhumbatira pauloyo nam'busu na mulayilana naye. 38 Makamaka adachita lisungu chifukwa cha mau yake yej onene kuti noo iwo sazamuanatcho nhope yake pambuyo adamupelekeza ku chombo.

Chapter 21

1 2 Ntawi imene tidaiana nao ndi tilipaulendo mnyanja, tidfika moja kwa moja mkati mwa muji wa kosi ndi siku lakawila lake tidafika mmoji wa Rodo, ndikuchokela kumeneko tidafika mmuji wa Patara. Yapo tidapeza sitima yoyomboka kupita Kufonike, tidakwela ndi kuendekela. 3 Yapotidafika pachogoro pa chilumba Kipro tidasia janja la kumanjele tida enda mpaka ku Siria tidaika chipumulizi pamoji wasilo chifuko kumeneko ndiko idalisitime ikwe zeke katundu wake. 4 Pambuyo pakwaona oyaluzidwa tidakale kumeneko masiku saba oyaruzidwa yawa adakambila Paulo kupitila mtima kuti iye siwaponda ku Yerusalemu. 5 Atapamenepo tidamalze masiku yaja ife tidachoka tidapita ulendo watu. Onche pamoji ndiocha akatu ndi wane watu adatipelekeze pakati panjila zetu tidaturuka kubwalo. Kubwalo kwa muji pambuyo tidagw maomono mpepete mwa nyanja, tidapempela, tidelailana ndi waliyenche. 6 Tidakwela sitime ukunaoncho atabwela mmiji mwaoncho. 7 Atayapo fido tela uleudo watu kuchokele kutilo tide fika kutolemai paja fide conjelawa ndi abale ndi kukale nao siku limoji. 8 Mawalake fide choka fide pita kukaisana ife tidalowa mnyumba ya Filipo olalikila mau la Mulungu uyo wadali mmoji wa anyi waja saba nafencho tidekale pamoji naye. 9 Muntu uyo wadali ndi ana mwali anai achamene adali osabalapo acha amene adaleta. 10 Pambuyo pakukala kumeneko kwa masiku yakuti wadachika kucho kela Kuuyahudi orofa mmoji watanidwa Agabo. 11 Iye wadaja kwatu ndi wadatenga lamba la Paulo chifuko wadaji manga miendo ndi manja yake mwenewake ndi kukamba, Mzimu Woyera wakamba chimwechi, "Wayahudi wa Kuyerusalemu sioa mmange muntu wamgwilirila lamba ili naoncho simpache mmanja mwa wantu ajiko." 12 Yapo tidavela nkani izi ife ndiwa amene amalama malo yaja tidampembeza Paulo siudakwela kupiita Kuyerusalemu. 13 Nde pamene wadayanka mchita chiyani mulela ndikuti dula mtima? Chifuko chamate ndili tayari usati kumangidwa chabe nampo kutera komweko Kuyerusalemu chifuko chajiona la Bwana Yesu. 14 Chifuko Paulo siwadafune kunanizidwa, tidasiane ndikukamba, "basi chikondi cha Mulungu chichefike." 15 Pambuyo pama siku yameneyo, tidatenga matumba yatu ndifita kwela Kuyerusalemu. 16 Moochepa mwa oyanzidwa wake kuchokela Kukaisaria naonche ada chatano nafe. Adaja naye mvute mmoji watanidwa Mnasomi muntu wa Kipro oyaluzidwa wakalemmene tide kala naye. 17 Yapo tidafika Kuyerusalemu abale adati landila kwa chikondi. 18 Siku la kawili lake Paulo wadapita pamoji nafe kwa Yakobo, ndikuwazee wonche adalipo. 19 Pambuyo pa kuwalonjela wada apacha nkani imoji mwaina ya nkani zimene Mlungu wadachita mkati mwa maiko kwa kuptila chitandizo chake. 20 Ntawi yapo adavela yameneyo anamkwezeka Mulungu, ndiada mkambila, "upenya abalewako kuli wantu wa anyinji akurupalila mkati mwa Wayahudi anyio wonche ali ndi chikurupalilo chogwila lamulo." 21 Akambilidwila kuchatana ndi iwe kuti uyaluza Wayahudi akale pakati miko kusiane ndi kuti wakambole kuti si adeatandize achi wana wao ndi siadafunafuna mwab wao wakale. 22 Ifunika tichite chiyani? Kapena pake kapena siavele kuti iwe wafika. 23 Mmwemo chita chija ifeti kukambila chapano tili ndi wantu anai ameni aika pangano. 24 Atenge achiwantu yawa ndi ujichuke wmwene pamoji ndi anyaiwo ndiuwa lipile vonche vimene atudikila dala kut akoze kumeta mitu yao mmwemo waliyenche nkani zimene akambidwa kupisila uwe ndi zaunami siayaluze kuti iwe nawencho uchata malamulo. 25 Nampo kwa nkani za wantu ajiko acha amene ali ochatila tidalemba ni kuchocha maagizo kuti afunika kujiika pampepete ndi vinthu vchochedwa chabilokela ndi chiati chapotedwa ndi ajiike pampepete ndi chigororo. 26 Ndi pawene Paulo wada atenga waachimuna ndi siku la kawili kujipembeza pamoji ndi anyiiwo wadalowa muhekalu ktangaza chipindi cha siku za kujipembeza mpakane sadaka ichochedwe chifuko cha waliyenche wao. 27 Siku zimene saba yapo zidawandikile Wayahudi ochepa kuchokela Kuasia adamuona Paulo muhekalu ndi ana kanyinji adakwiya ndi kumkwezela maya. 28 Adali ndi ameinya pokoso "wanthu wa Kuiziraeli, mtitangatileuyu nde yuja wa ayalua wanthu pamalo pali ponche nkani zimene zili kumbuyo ndi wanthu, lamulo, pamalo pano sonincho wanjanao Wayunani pakatikaty pa nyumba ya mapempelo ndi kupachita ukazuzu pamalo pano pali malo ya bwino." 29 Pakuti poyamba adamuona Trofilo Muefesowali pamoji nao mumuji, naoncho ameaganiza kuti Paulo wadaja naye mmalo mapempelela. 30 Muji wonche udali ndi walowa pokoso, ndi wanthu adatawa pamoji ndi kumgawira Paulo, adamchocha kubwalo cheko kamoji vidamangidwa. 31 Yapo amayesa kufuna kumpa nkani zidamfikila wamkuru wazankondo la ochekeleza Muyerusalemu yonche idalowa mtimbwilikanyo. 32 Ntawi yomweyo wada atenga azankondo ndi wamkuru wazankondo wadalitamangila guru, ntawi wantu yapo adamuona wanikuru wa zankondo ndi asirikali wake, adasia kumtimba Paulo. 33 Pambuyo pake wamkuru wa zaukondo wadamsedelea ndi kumgwira PAulo ndi kulamula wamangidwe vingwe vya chichulo viwili. Wadamfuncha iye ndiyani ndi wachita chiyani. 34 Wantu ochepa mkati mwa guru amango kambakamba wena akamba ichi wena akamba icho. Pakuti wambile chilichonche kifuko cha yaya mapokoso wadalamula Paulo wapelekedwe nyumba ya malamulo. 35 Kusia chimenecho yapo wadafika pa makwelelo wadatengedwa ndi azankondo chifuko chamtimbwilikanyo wawantu. 36 Chifuko guru la wantu adamchata ndi adaendekela kubula mapokoso, "mchocheni uyu." 37 Paulo yapo wamapelekedwa mkati mwa nyumba ya malamulo, "wadamkambila wamkuru wazankondo" ndikoza kukukambila chinthu? Yuja wamkuru wazankodo wadakamba, "bwanji ukamba Kiyunani?" 38 Bwanji iwe osati yuja Mmisri poyamba wadachogoze kwakila ndi wadaatenga oukila elfu ne ntengo?'' 39 Paulo wadanena, "ine Muyahudi, kuchokela muji wa Tarso ya Kilikia. Ine ndili mmoji wajiko lojiwika nikukupempani mundilole ndikambe ndi wantu." 40 Ntawi wamkulu wazankondo yapo wadampaja lamulo Paulo wadaine pamakwelelo ndikuchocha chilangizo kwa wanthu kwa janja lake, ntawi yapo kudakala kachete kupunda, wadakamba nao kwa Kihebrania. Wadakamba,

Chapter 22

1 Abale ndi acha atate wanga vechelani chitetezi changa siniichichite kwanu chipano. 2 Ansoghano yapoadavela Paulo ndi wanena nawo kwa Chiebrania adakala chete. Kunena, 3 "Ine ndi Myahudi, nabadwa mujhi wa Tarso malo la Kilikia nampho nidapata mayaluzo pa mujhi uuni, pamyendo pa Gamalieli. Nidayaluzidwa kulingana ndi njila zene za matauko za atate wantu. Ine ndili ni jhitajhita ya Mulungu, ngati anyiimwe mwawonche umo muli lelo. 4 Nidekupwetekani kwa njila iyi mpakana kufai nidakumangani wachimuna ndi wachikazi ndi kukutayani mndende. 5 Ata wamkulu wa nchembe ndi midala wonche akoza kuchocha umboni kutinidalandila kalata kuchoka kwaiwo kwa chifuko cha abale li kudameski kwa ine kusafiri kupila kumeneko idali nikupelekeleni wanthu kuyerusalemu kwa njila ijha kuji omangidwa avutichidwe. 6 Idachovela kuti pajha nidali paulendo kuwandikila ku dameski nyengo za usana chizulumukila ndangalila lalikulu lidachokela kumwamba idayamba kunimulika. 7 Nidagwa panchi ndi kuvela mau kunikalubila sauli sauli chifukochanji uvidanda ulicha. 8 Nidayankha, "iwe ndi yani atate?" wadanikambila , "ine ndi yesu mnazereti nyo ine umdaulicha.' 9 Anyiwajha adali ndi ine adaona adangalila, nampho siadavele mau yayujha uyo wadanena ndi ine. 10 Nidanena, nichite chiyani, Atate? Atate adanikambila, "ima ndi ulowe Kudameski; kumeneko siukamblidwe kila chindhu ufunika kuchita." 11 Sinidakoze kupenya lava ndende ya mwangaza wa dangalila lijha, ndipo nidapita kudameski kwa kuchogo lelendwa ndi manja ya anyiwajha adali ndi ine. 12 Kumeneko nidakomana ndi mundhu watanidwa Anania wadali mundhu uyo wadagwila matauko ndi mwene kulemekezeka pachogolo pa Wayahudi amakala kumeneko. 13 Wadajha kwa ine, wadaima pachogolo panga, ndi kunena, mbale wanga Sauli, upeze kupenya: kwa ntawi imweijha nidamwona. 14 Adanena mulungu wa Atate watu wakusagula iwe upeze kujhiwa chikondi chake, kumwona yujha mwene chilungamo, ndi kuvela mau yachoka pakamwa pake. 15 Kwa ndande siukale mboni kwiye kwa wandhu wonche pamwamba pa yayowayaona ndi kuvela. 16 Mmwemo chipano kwa chiyani unilindilila? Ima, abatizidwe, ukachukidwe machimo yako, ndi ulitana jhina la iye.' 17 Pambuyo pa kubwela Kuyerusalemu, yapo nidali ndinipembhela mkati mwa nyumba yopembhela, idachokela kuti napachidwa maloso. 18 Nidamuona niwanikamila chichimichimi uchoke Kuyerusalemu msanga, kwa ndande siavomela umboni waiwe kukuza ine.' 19 Nidakanena Atate anyiiwo achinawene ajhiwa nidaamang'a mudende ndi lawa menya anyiwajha adakulupalila pa masinagogi. 20 Ndi mwazi wa Stefano mmboni wa iwe yapo idamwazika, ine nane nidali naima powandikila ndi kuvomela ndi nidali ndisunga nchalu za anyiwajha adampha. 21 Nampho adanikambila, "mapita kwa ndande ine sinikutume upite papatali kwa wandhu ajhiko." 22 Wandhu adampacha lamulo akambe pamwamba pa maunli. Nampho pambuyo adakuzi mau ndi kunena, "mchoche mundhu uyu pa jhiko; kwa ndande osati zene walame." 23 Yapo wadakuza mau ndi kumtangatila vovala volwo ndi kutaya malifumbi kumwamba. 24 Jemedali wamkulu wadalamula Paulo wapelekedwe mnyumba, wadalamula wafunchidwe pamwepo ndi watimbidwa vichailo, kuti iye mwene wajhiwe kwa chiyani wadali kumtimbila mapokoso ntundu ujha. 25 Ata yapowadali ammanga kwa maluzi, Paulo ademkambila yuja akide wada ima kuwandikilana ndi iye, Bwanji ni malinga kwanu kumtimba mundhu wali Mrumi ndi wakali kulamulidwa? 26 Yujha akida yapo wavaela mau yajha, wadapita kwa jemadari wamkulu ndi kumkambila kunena' "ufuna kuchita chiyani? Kwa mate mundhu uyu ndi Mrumi." 27 Jemedari wa mkulu adajha ndi kumkambila, "niambile, bwanji iwe ndi wa mujhi wa Kurumi?" Paulo wadanena, yetu. 29 Jemedari wadayankha, "ndi kupitila unyinji za ndalama ndipo ndidapeza." Nampho Paulo adamkambila, "ine ndi Mrumi wa kubadwa." 28 Basi anyiwajha adali tayari kupita kumfucha adachoka ndi kumsiya nyeno imweijha. Ndi jemedari naye wadawopa, yapo wadajhiwa kuti Paulo ndi Mrumi, ndi kwa ndande wamwanga. 30 Siku idachatila, Jemedari wamkulu wadafuna kujhiwa uzene kukuza milandu ya Wayahudi kupunda ya Paulo. Chimwecho adammasula vilunjo vake wadalamula wamkulu wa nchembe ndi bwalo lonche apezane. Adampeleka Paulo panchi ndi kumwika pakatipakati pawo.

Chapter 23

1 Paulo wdaapenyesha wanthu a baraza ndi kuakambila, abale wanga ndakala ndikufunila za bwino mbaka lelo pamaso pa Mulungu. 2 Wamkulu wa anchembe, Anania wadaalamula anyiwaja adima pafupi ndiiye am'bule kukamwa kwake. 3 Paulo wadamkambila, "Mulungu siwakubulelwe, pupa lanyekedwa, wakala unilanga kwa tauko ndi ulamula nibulidwe pasachata tauko?" 4 Anyiwaja adaima pafupi ndi iye adakamba chimwechi nde umo umtukwanila wamkulu wa nchembe wa Mulungu? 5 Paulo wadakamba, "achiabale wanga ine sinidajiwe kuti uyu wamkulu wa nchembe. Pakuti yalembedwa, siukamba kuipa kwa oimilila wanthu wako." 6 Paulo yapo wadaona pa gulu lija kuli Afarisayo ndi Asadukayo, wadakamba kwa mphavu achiabale wanga ine ndi Mfarisayo mwana wa Mfarisayo, napelekedwa pa koti chifukwa ndikulupilila akufa sahyuchidwe. 7 Yapo wadakamba chimwechi ndeo idachokela kwa Asadukayo ndi msonkhano udasweka. 8 Ndande Asadukayo akamba kulibe kuhyuchidwa, palibe angelo, palibe mzimu, nampho Afarisayo akamba voncheo vilipo. 9 Ndeo yaikulu idachokela, akumoji wa olemba wa Afarisayo, adaima ndi kukamba sitidachionechoipa kwa munthu uyu, bwanji, pena mzimu, kapena angelo acheza ndi iye? 10 Ndeo idapunda kukala yaikulu, wamkulu wa asirikali wadaopa kuti Paulo angamng'ambeng'ambe kwa icho wadaalamula asirikali wake kulwelela gulu lija ndi kumchocha Paulo ndi kum'bweza mkati. 11 Usiku udachatila Ambuye adaima pafupi ndi Paulo adamkambila, "usaopa, wanichitila umboni mu Yeruslemu, ndi Kuroma nako ukachocha umboni wanga." 12 Yapo kudacha akumoji mwa Ayuda adajiikila chileso achinawene kuti sitidya ndi stimwa chilichonche m'baka yapo sitimpe Paulo. 13 Kudali ndi wanthu oposa makumi anai amapanga khani imeneyi. 14 Adapita kw waakulu anchembe ndi kukamba tajiika tawefe mchileso chachikulu kuti, "tisa dadya chilichonche m'baka timpe Paulo. 15 Kwaicho baraza limkambile wamkulu wa asirikali wakamtenge waje nayo kwa anyiimwe kuti mkuja kulamula mlandu wake mwawe kuti mkuja kulamula mlandu wake mwa malinga ife tajikonja kumpa wakali osafike pano." 16 NAmpho mwana wa m'bale wake Paulo wadavela mauyo, kwa icho wadalowa mkati ndi kumkambila Paulo. 17 Paulo wadamtana mmoi wa asirikali ndi kumkambila, "mtenge mnyamatayu mpeleke kwa wamkulu wa asirikali wali ni mau wafuna kumkambila." 18 Msirikal yuja wadamtenga mnyamata ndi kumpela kwa wamkulu wa asirikali ndi kumkambila, PAulo yuja wamangidwa wadanitana ndi kunikambila nimpeleke mnyamatayu kwa iwe wali ndi mau ya kukukambila. 19 Yuja wamkulu wadamgwila pajanja ndi kupita nae pamphepete, ndi kumfuncha, chinthu chanji ufuna kunikambila?'' 20 Mnyamata yuja wadakamba, Ayuda avana kukupempha, ujenayo Paulo mawa pa baraza ngati afuna kujiwa nkhani zake. 21 Kwa icho iwe uadavomela ndande wanthu makumi yanai, ajiikila chileso kuti saadya ndi saamwa mbaka ampe Paulo, chipano andolindila lamulo kuchoka kwa iwe.'' 22 Yuja wamkulu wa asirikali wadamsiya mnyamata ndi kumkambila siwadamkambila munthu wali yonche kuti wanikambila nkhani ii. 23 Waatana asirikali awili ndi kuakambila ikani asirikali okwela bulu ndi ali ndi nthungo simchoke zamu ya katatu usiku. 24 Ikhani viyama wadakwele Paulo, mufikiche bwino kwa Feliki wamkulu wa chigao. 25 Wadalemba karata kwa mtundu uu. 26 Klaudio Lisia kwa wamkulu wa chigao Feliki, moni. 27 Munthuyu wadagwilidwa ndi Ayuda adali pafupi kumpa nde nidapita pamoji ndi asirikali nidampulumucha, yapo nidavela kuti iye ndi Mroma. 28 Nidafuna kujiwa ndande chiyani amuimba mlandu, kwa icho nidampeleka kubaraza. 29 Nidaona kuti wadaimbidwa mlandu chifukwa cha mafuncho ya matauko yao, ndi siwaadaimbidwe mlandu ndi mau lililonche lienela kupedwa kapena kumangidwa. 30 Kenaka idajiwika kuti kudali chisisi chimafuno kuchitika kwa iyeyo, mwa msanga nidamtuma kwanu. Nidaakamba yao amuimba mlandu apeleke mlandu wake pamaso panu, adalailana.'' 31 Anyiwaja asirikali adavomela lamulo, adamtenga Paulo ndi kumpeleka ku Antipatri usiku. 32 Siku lidachatila, asiriki ambili adaasiya okwela bulu apite pamoji ndi iye, anyiiwo adabwela. 33 Ndi okwela bulu yapoadafika ku Kaisaria, ndikumpacha wamkulu wa chigao karata ija, adamuika Paulo pamaso pake. 34 Wamkulu wa chigao yapo wadaisoma karata, wadamfuncha Paulo wadachokela chigao chiti, yapo wadajiwa kuti ni munthu wa Kukilikia. 35 Wadakamba sinikuvele iwe yapo saaje anyiawo akuimba mlandu, wadalamula waikidwe mnyumba ya chigao ya Herode.

Chapter 24

1 Pambuyo pa masiku yasano, Anania kuhani wamkulu, wina wake wa Okota ndi akamba mmojhi wataniwa Tertulo, adapita pajha. Wanthu yawa apeleka milandu pakati pa Paulo. 2 Paulo yapowadima pachogolo pa gavana, Tertulo wadayamba kumuimba milandu ndi kukamba kwa gavana, "kwa chifuko chako tili ndi mtendele waukulu, ndi kupenya kwako kuapeleka kung'anamuka kwa bwino pakati pa jhiko lathu, 3 Basi kwa kuyamikila konche tilandila kila chinthu icho uchichita, kwamoni olemekezeka Feliki. 4 Nampho sinidakulemecha kupunda nikupempha univechele mau yochepa kwa. 5 Kwa mate tampata munthu uyu wandeo, ndi wachiticha Ayahudi onche kupanduka pajhiko. Tena ni ochogoza madhehebu ya anazorayo. (penyelela mau ya mzele uu 24:6 6 Ndi tena wadaesa kulithila hekal azi chimwechotidamgwila; palibemo mnakala za bwino za kale). (Penyelela mzele uu 7 Lisiasi, afisa, wadaja ndi kumtenga kwa mphavu mmanja mwathu, palibema mnakala za bwino za malembo ya kale.) 8 Ukamfuncha Paulo kukhuza vinthu ivi, ata siukhoze ujhiyaluza ni chinthu chajhi tamuweluzila. 9 Ayahudi nao adamuweluza Paulo, naakamba kuti ivi vinthu vidali va zene. 10 Liwali wadamkwezela jhanja kuti Paulo wakambe, Paulo wadayankha, "nijhiwa kuti kwa vyaka va mbili uli olamula wa jhiko lino, ndi nili ndi chisangalalo kujhikambilila namwene kwako." 11 Ukhoza kuhakilisha kuti sizidafike masiku kupitilila maiku kumi ndi ziwili kuyambila yapo nidakwela kupita kumtamanda Kuyerusalemu. 12 Ndi yapo adanipeza pahekalu, sinidachuchane ndi mnthu waliyonche, ndi sinidachite ndeo pakati pa msonkhano, wala pamasinagogi wala mkati mwa mujhi. 13 Ndi wala sakhoza kuhakikisha kwako maweluzo yayoyaweluza pakati panga. 14 Nampho nivomela ili kwako, yakuti kwa njila nimtumikila Mulungu wa achaatate wathu. Ine ndi okhulupilila kwa yaliyonche yali mthauko ndin malembo ya olosa. 15 Nili ndi ujasili umweujha kwa Mulungu uoata anyiwajha nao uo aulindilila, kujha kwa kuhyuka kwa akufa, kwa onche wene haki ndi opande haki. 16 Ndi kwa ili nichita nchito kuti nikhale ndi dhamira ilibe hatia pamaso pa Mulungu ndi pamaso pa wanthu kupitila vinthu vonche. 17 Chipano pamalo pa vyaka vambili najha kupeleka mthandizo kwa jhiko langa ndi mphaso ya ndalama. 18 Yapo nidachita chimwechi, Ayahudi akuti a Kuasia adanikomana mkati mwa chisngalalo chochukidwa mkati mwa hekalu, popande gulu la wanthu wala chipwilikiti. 19 Wanthu yawa yao ifuika kukhalapo pachogolo pako chipano ndi akambe chijha alinacho pakati panga ngati ali ndi mau lalilonche. 20 Kapena wanthu yawa achinawene akambe kulakwa kwanji uo akuona kwanga yaponidaima pachogo pa bwalo la Kiyahudi. 21 Ingakale kwa chinthu chimojhi ichonachikamba kwa mau yaponidaima pakatikati ao, ni kwa chifuko cha kuhyuka kwa akufa anyiimwe, "munilamula" 22 Feliki wadapachidw nkhani bwino kukhuza njila ndi wadaubwezecha msonkhano.wadakamba ''lisia jemedali yapo siwajhe panchi kuchokela Yerusalemu sinichoche lamulo pakati pa maweluzo yanu''. 23 Ndeyapo wadalamula akida wampenyelele paulo nampho wakhale ndi siwadakhalapo munthu wa kwaaniza mabwenji yake asadamthangatila wala kumuendela. 24 Pambuyo pa siku za kutifeliki wadabwela ndi drusila mkazake uyo wadali muyahudi adatuma kumtana paulo ndi kuvechela kuchoka kwa iye nkhani za chikhulupi mkati mwa kristo yesu. 25 Nampo Paulo yapowama kukambilana nae khuza haki, kukhala ndi kiasi ndi lamulo ilo silihe, feliki wadapata mantha wadayankha, pita kwakutali kwa chipano, nampho nikapaata nyengoncho, sinikutane." 26 Nyengo imueyo, wadakhulupalila kti paulo siwampache ndalama kwa chimwecho wadamtana mala kambili wadakambana nae. 27 Nampho vyaka viwili yapo vidatha, prokio festo wadali liwali pamalopa feliki, nampho faliki wadafuna kujhisendeza kwa ayahudi, chimwecho wadamsiya paulo panchi pa kupenyeleledwa.

Chapter 25

1 Ndiyapo festo yapowadalowa katika hekalu lijha ndi phambuyo pasiku zitatu wadapita kuchoka kaisalia hadi kuyerusalemu. 2 Kuhani wamkulu ndi wayahudi mashuhuli adapeleka lawama dhidi yapaulo kulafesto ndi adakhamba kwa mphavu kwa festo. 3 Ndi adamphempha festo fadhili pamwamba pa nkhani zapaulo wapheze kumtana kuyelusalemu iliakoze kumpha mnjila. 4 Nampho Festo wadayankha kuti Paulo wadali omangidwa kaika Kaisali, ndi kuti iye mwene siwabwele kumene chisangu. 5 Wadakamba, "kwachimwecho, anjiwajha ambao akhoza kupita kumene ndi ife, ngati kuli chintu choipa kwa muntu uyu, mfunika umshitaki." 6 Pambayo pokala siku nane au kumi zaidi,wadabwela kukaisalia ndi siku lidachatha wadakhala phamphando wa kulamulidwa ndi kumlamula paulo wapelekedwe kwoke. 7 Yapoadafika Wayahudi kuchoka Kuyerusalemu adaima pafuphi, adachocha malalamiko yambili yolemela amayo siadakoze kuyahakikisha. 8 Paulo wadajitetea ndi kukamba, sizidi la jina la Wayahudi, si pamwamba pahekalu, ndi si pamwamba pa Kaisari, nachita voipha.' 9 Nampho Festo wamafuna kujipendekeza ka Wayahudi, ndi chimwecho wadayanka Paulo kwakukamba, bwa ufuna kupita Kuyerusalemu ndi kuhukumidwa ndi ine kupitila vintu ihi kumeneko? 10 Paulo wadakamba, niima pachogolo pamphando wa lamulo la Kaisali ambapo nifunika kuhukumidwa. Sindidawalakwile Wayahudi, ngatiiwe umoujiwila bwino. 11 Ikakala nalakulila ndi ngati nachita ichochifunika nyifa, sinikana kufa nampho ngati lawama zao sikantu, palibe muntu wako za kunikabizi kwao, nimpempha kaisari." 12 Baada ya Festo kukamba ndi baraza wadayanka," umpepha kaisari, udapite kwa kaisari.'' 13 Baada ya siku zingapu, Mflume Agripa ndi Bernike adafika kaisari kuchita ziara lasmi kwa Festo. 14 Baada ya kukala pamepo kwa ntauli yambili, Festo wadapeleka milaundu ya paulo kwa mflume wadakamba, muntu mmoji wadasidwa pano ndi Feliki ngati omangidwa. 15 Yaponidali kuyerusalemu makuhani waakuluakulu ndi wazee wa Wayahudi adapeleka malalamiko pakati pa muntu uyu kwanga' nao adafucha pakati pa hukumu zidi yake. 16 Kwaili ine nida yanka kuti si desturi ya roma kumchocha muntu kwa upendeleo badala yake, ohukumidwa ifunika kukala ndi nafasi ya kuwakabili oshitakidwa wake ndi kujitetea kupitila tuhuma zimene. 17 Kwachimuecho, Yapoadaja pamoji pano, sinidakoze kulindilila, nampho siku lidachata nidaka papando pahukumu ndi kulamula muntu uyu wapelekedwe mkati. 18 Nyendo oshitaki yapoadaima ndi kumstaki, nidaganizila kuti palibe mashtaka yayakuluyayo yapelekedwa zidi yake. 19 Pambuyo pake, adali ndi mabishano fulani amoji nae kuhusu dini yao ndi kuhusu Yesu ambaye wadali wafa, nampho Paulo wadai kuti wamoyo. 20 Nidali namangidwa jinsi ya kupenya sala ili, ndi nidamfucha ngati walakapita Kuyerusalemu kuhukumidwa kuhusu vintu hivi. 22 Nampho Paulo yapowadatanidwa waikidwe chini ya ulizi kwa chifuko cha maamuzi ya mflume, nidalamula waikidwe mpaka yaposinimpeleke kwa kaisari. 21 Agripa wadakambana ndi Festo ,"nikadakonda kumvechela muntu uyu."Festo wadakamba,"mawa siumve chele.'' 23 Chimuecho mawa lake. Agripa ndi Bernike adafika ndi sherehe yambili, adafika kuukumbi ndi mafuru akijeshi, ndi mafuru akijeshi, ndi wantu mashuhuri ajiko, ndi Festo yapowadachocha maramulo, Paulo wadapelekedwa kwao. 24 Festo wadakamba," mfulme Agripa, ndi wantu onche ambao mlipo pano pamoji nafe, mumuona muntu uyyu, jumuiya yonche yawayahudi kumene kuyerusalemu ndipano afuma nashauri , ndi nao adatimba kelele kwanga kuti siwadaishi. 25 Ndidaonaona kuti siwadachite chalichonche listahili nyifa, nampho kwa chifuko amtana mfulme, nidalamula kumpeleka kwake. 26 Nampho nilibe chintu chamate cha kulemba kwa mfulme, kwa chifuko ii, nampeleka kwake, hasa kwako iwe. Mfulme Agripa, ili nipeze kukala ndi chintu cha kulembe kuhusu milandu. 27 Pakuti ndiona ilibe mate kumpeleka omangindwa ndi bila kulangiza mashitaka yayoyamfuna.

Chapter 26

1 Basi Angripa wadamkambila Paulo upachidwa kunjika mbilila ndo Paulo wadanyoshe janja lake kunjikambilila chimwe. 2 Najiona nilini kukondwa mfumu Agripa dala kuchila mlandu wanga pachogolo pako lelo zidi ya malakamo yonchhe ya Wayahudi. 3 Hasa kwa ndondi iwe onjwa wa ukalo wa Wayaudini mayunchho chimwechi nipempha umvechele. 4 Zene Ayahudi onchhe ajiwa umo na lamila tangu unyamata wanga katika jiko langa kuja Kuyerusalemu. 5 Amjewa tangia kumayambo ni mfunika kuvomela kuti mikala ngati Mfarisayo, kanisa ni msimama waukulu kudini yatu. 6 Chapano naima nilamulidwe kwa ndamole ine nidapenya pangano ambalo mlungu wadachita wa achatawatu. 7 Ili ni pangano ambalo mafuko yatu kumi na mbili ya kupalila uulandila ngati yamgwadile Mulungu kwa kujituma usiku ni usoma.Ni kwa ajili ya kulupalilo ili, Mfumu Agripa, kuti Ayahudi amimba mlandu. 8 Kwa ndonde chiani walionehhe waganizila ni lodabicha kuti Mulungu wamyhusha wafa? 9 Nthawi imoji mdaganizila na mwene kuti mdakachita mambo ya mbili zidi ya jina mpulumusi wa Nazareti. 10 Nidachita yaya katika Yerusalemu Nidamonga okulupalila ambili mndende ni nidali ni malamulo kuchoka kwa wakulu akulu anchembe kuchila chimwecho ni nthawi amapedwa nidabula chidindo zidi yao. 11 Mara za mbili nidabula katika umo apemphela monchile ni nidaesa kwa chita akane chikulupi chao. Nidali ni hasira kupunda pamwamba pao ni nidatopola ata katika miji ya kuchilendo. 12 Nthawi yapo mimachila yaya,midapita kudameski,nikakala ni malumulo nikakala nimalumulo nimalangizo kuchoka kwa wakulu amehhembe; 13 Yapo nidali mnjila nthawi ya usana,mfumu,nidaona domgalile kuchoka kumwamba lidali likalikuliko jua ni lidawala uuzungulila ine ni wamthu anyiyao amasafiri pamoji ni ine. 14 Ife taonchhe yapo tidagwa ponchhi, midavela sauti imaliamba ni ine imakamba kwa mkambo wa kiebramia 'sauli, sauli! ndande chiami unizunja? nikulimba kwa iwe kuubula teki mchokoo. 15 Nde yapo nidakomnba"Iwe ni yami; Ambuye? Ambuye adayankho, ine ni Mpulumusi iye unizunja. 16 Chapano inuka uime kwa myendo yako; ndonde kwa dala ili ine naonekana kwa iwe, nakusankhe ukale otumina ni mboni juu ya vichito ivo ujiwa kuhusu ine chapomo ni vichito nikulangize pambuyo. 17 Ni nikuombole kuchoka kwa wamthu ni wamthu anaakamu yapo nikutuma. 18 Kuchakula maso yao ni kwa choche kumdime kupita kuli domgalile kuchoka kuli nkhongono za satano amngomamukile Mulungu; daila apate kulandila kuchoka kwa Mulungu lekelelo la chimo ni chositidwa icho mwapachidwa anywaja adachochedwa kwa chikulupi chili liwonga. 19 Kwa icho, mfumu.Agripa, sinidakoze kulakwa maganizo ya kumwamba. 20 Nampo, kwa amyiyao ali Kudameski poyomba, ni tena Kuyerusalemu ni jiko lonche la yudea, ni pia kuli wamthu amaiko ina, nidalalikila kutialape ni kumng'omamukila Mulungu, achite vichito vikozekome kulapa. 21 Kwa ndande imeneyo Wayahudi adanigwila mkamisa adaesa kunipa. 22 Mulungu wadanitongatila mpaka saino, chimweshi niima ni uzene kwa wamthu akawaida ni kwa anyiwaja wakulu juu ya yaja ambayo openya patali ni Musa adakomba yachokele ni osati vino. 23 Kuti Mpulumusi lazima wazunjindwe ni siwakale oyamba kuhyushindwa kuchoka kwa akufa ni kutangazila dangalila kwa Wayahudi ni wamthu amaiko. 24 Paulo wadamaliza kujikambilila, Festo wadakambakwa sauti yaikulu ; Paulo, iwe ni opambwane! Mayaluzo yako yakuchita ukale opombwane. 25 Nampho wadakomba, ineosali opambwane olemekezedwa Festo nampho kwa kuji kulupalila ni komba mauya uzene okaoka. 26 Pakuti mfumu wajiwe kuhusu vichilo hivi ni chimwecho ni Komba kwa uwazi wake kwa maana mlimi uhakika kuti paliji lalitonehhe labisidwa kwa iye;pakuti ili lidaitidwe pamphepete. 27 je ukulupalile openya paehogolo mfumu agripa mjiwa kuti ukulupalila. 28 Agripa wadamkambila Paulo kwa nthawi pa itupi ukofa kumguzoine mkumchita okulupalila? 29 Paulo wadakamba "nimpemphe Mulungu kuti kwa nthawi pa itupi au yaifali asatiiwepe bali kuti onchhe anivela lelo akalengatiine nampho poponda minyororo ya kundende." 30 Ndipo mfumu wadaima ni liwali ni Bernike nae ni anyiwaja adali akala pamoji ni anyiio 31 Yapoadachoka kochezela adakambilo anyiio ni kukamba munthu uyu siifunika nyifa wala kumongidwa 32 Agripa wadamkambila Festo ''munthu uyu wadakakoza kukala osililidwa ngati siwadakadula kupita mehogolo kwa Kaisari.''

Chapter 27

1 Yapo idalamulidwa kuti tufunikana kusafiri kwa maji kupita Kuitalia adamkabidhi Paulo ndi amangidwa winancho kwa afisa mmoji wa jeshi la Kiroma uyowadatanidwa Julio, akikasi cha Agustani. 2 Tudakwela meli kuchoka Kuadramitamu, iyo imasafiri mphepete mwa Asia. Mchimwecho tudalewa mnyanja Aristaka kuchoka Kuthesolanike ya Makedania wadapita pamaji nafe. 3 Siku idachotela tudatila nanga pakati pa muji wa Sidoni, yapo Julio wadamchitila Paulo kwa kumlandila ndi wadamruhusu kupita kwa achabwenji wake kulandila chikondi chake. 4 Kuchoka pamenepo tudapita kunyanja tudasafiri kuzungurila kisiwa cha Kipro icho chidakinga mphepo, chifukwa mphepo imato tusumbua. 5 Baada ya kusafiri pakati pamaji yalikalibu ndikilikia ndi Pamfilia ,tudaja kumira, muji wa Lisia. 6 Paja yuja afisa wa jeshi la Kiroma, wadaipela moli kuchoka Kualexandria iyo imasafirikupita Kuitalia wadatukwela mkati mwake. 7 Baada ya kusafiri pang'onapang'ono kwa siku za mbili ndi badaye tudafika kwa taabu karibu ndi Kinidasi, mphepo siidalolezencho kuelekea njila imeneyo, mchimwecho tudasafiri mphepete mwa mtunchi wa Krete ndi tu kinga mphepo, mkabala ndi Salmone. 8 Tudasafiri mphepeto mwa nyanja kwa ugumu, mpaka tudafika pamalo patanidwa Fari Haveni iyo ili karibu ndi mji wa Lasi. 9 Tudatenga nthawi ya mbili sana, ndi nthawi ya kumanga kwa Wayahudi adapitancho ndi chipana idali ndi hatari kuendelea kusafiri mchimwecha Paulo wadatuonya. 10 Ndi kukamba , ''wachimuna, ndiona safari ambaya tu tuitenge siikale ndi madhara ndi asara yambili asatipe ya mizigo ila ndi chombo nampho ndi umoyo watu". 11 Nampho afisa wa jeshi la Kiroma wadamvechela zaidi mbuye wake ndi olamula wa chombo kuliko vinthu vija ambavo vidakambidwa ndi Paulo. 12 Kwa chifukwa dooka sidakale pamalo pa rahisi kukala nyongo ya kuzizila ogwila nchito msitima ambili adashauri tusafiri kuchoka paja, ili kwa namna yaliyonche tukakoza kufika muji wa Foinike, tukale paja nyengo ya kuzizila, Foinike ndi dooke kumeneka Kukrete, ndi ipenya Kaskazini Mashariki ndi Kusini Mashariki. 13 Mphepo ya Kusini yapoidayamba kuvuma pang'ono pang'ono, ogwila nchito msitima adaganizila apata chija amachifuuna adazula nanga ndi kusafiri mphepete mwa Krete karibu ndi. 14 Namphe baada ya nthawi ya ifupi mphepo ya mphavu, uwadatanidwa wa kaskazini mashariki, udayamba kutubula kuchoka chijala. 15 Nyengo chembe yapochidalemeledwa ndi hali himeneyo, tudasafirishidwa ndiie. 16 Tudatawa kupikila lija bendeka ilo limakinga mphepo ya bwani itanidwa kauda; ndi kwa taabu sana tudakeza kulamicha bwato. 17 Baada ya kuigula, adatumialuzi kuimanga chambe, adaepa kuti adakakeza kupita kumalo kwa mchenga wambili wa syiti, mchimwecha adachicha nanga ndi adaendechedwa pang'onapang'ona. 18 Tudabulidwa kwa mphavu sana ndi mwela, mchimwela siku iyoidachotela ogwila nchi tamsitima adayamba kutaya mizigo kuchoka mchembe. 19 Siku ya katatu, ogwi la nchita msitima adayamba kuyachacha maji kwa manja yae achinawene. 20 Nyengo yape jua ndi nthendwa sizida tuwalile kwa kwa siku zambili, bado mwela waukulu udatubula, ndi chikhulupi kuti tudakalamichidwa idacheka. 21 Baada ya kuti apita kwa nthawi ya itari bila chakudya, pamenepo Paulo wadaima pakati pao gwilanchito msitima wadakamba, "wachimuna idabidi mnivele, ndi sitidaka zula nanga kucheka Krete, ili kupata yaya madhara ndi hasara. 22 Ndi chipano ndikupemphani mgwile mtima, kwa chifukwa sikukala ndi kutaika kwa umoge mkati mwanu, ingakale hasara ya chembepe. 23 Kwa chifukwa usiku uweudapita angale Amulungu, ambaye, mmeneyo mulunguine ndi wake ,ndi uyo ndi mgwadila angela wake wadaima mphepete panga. 24 Ndi kukamba, "usaepa Paulo. Lazima uime pachogola pa Kaisari ndi ponya, Mulungu mkati mwa ubwina wake wakunikha anyizawa anche ambao asafiri pamaji nawe. 25 Mchimwecho, wachimuna limbani mtima, kwa chifukwa ndimkhulupalila Mulungu, kuti siikale ngati umona kambidwila. 26 Nampho lazima tupwetekedwe ka kubulidwa pakati pa baadhi ya madooko." 27 Yapo udafika usiku wa kumi na nne, yapatumandechewa kumeneke ndikumeneko ku nyanja ya Adratiki ngati usiku wa manane mchimwechi agwilanchita msitima adaganizila kuti akaribia pamtunda. 28 Adatumia milio kupimila kunyoa kwa maji ndi adapata mita thelathini na sita, baada ya nyengo yayifupi adapi mancho adapata mita ishilini na saba. 29 Adaapa huti tukoza kuganga myala, mchimwecho adachicha nanga zinai kuchoka pakati pa sehemu yeika nanga zinai kuchoka pakati pa sehemu yaika nanga ndi adapempha kuti umawa udakaja mapema. 30 Anyiwaja ongila nchita msitima amafu nafu na namna ya kuisia chambo ndi adazichicha mmaji zibwato zazing'onozing'ono za kulamichila umoyo, ndi adajichita kuti atayananga kuchoka pamalo papachogolo pa bwate. 31 Nampho Paulo wadamkambila yaja asikari wa jeshi la Kiroma ndi anyiwaja asikari, "simkoza kulamicha ingakale anyiyawa wanthu abaki mchamba. 32 Ndeyapo anyiwaja askari adadula vingwe va uja bwato ndi udasiidwa utengedwe ndi maji. 33 Nyengo dangalila a umawa yapelima chokela, Paulo wadaapimpha anche angalau adye kidogo, wadakamba,ii ndi siku ya kumi na nne mulindila bila kudya, simdadye chinthu. 34 Mchimwecho ndi kupemphani mtenge cha kudya pang'ana, kwa chifu kwa ii ndi kwandande ya umeyo wanu,ndi palibe ata chichi limaji la mmutu mwanu uosiutaike. 35 Yapo wadatokamba yameneyo, wadatenga mkate wadayamikila Mulungu pachogolo pamaso ya kila munthu, ndeyapo wadaumeze mkate wadayamba kudya. 36 Ndeyapo onche adagwila mtima ndi nao adatega chakudya. 37 Tudali wanthu 276 mkati mwa chembe. 38 Yapo adato kudya vakudya va kutosha, adachita chamba chiepuke kwa kutaya ngane mkati mwa nyanja. 39 Yapa idali usana siadajiwe pamtunda nampho adaona pamalo papamtunda ijapo padalewa mmaji iyoidali ndi mchenga wambili, adafotokezelana ngati akaza kuchiendecha chembe kuelekea pamenepo. 40 Mchimwecho adazilegeza nanga adazisia mnyanja pakati pa nyengo imweyecha adalegeza vingwe za tanga ndi adainua malo ya pachogolo kuelekea kumphepo, mchimwecho adaelekea kumeneka kumalo kwa nchenga wambili. 41 Nampho adaja pamalo ambapo myeeza iwili ya mmoji ipezana, ndi chamba chidaelekea kumchenga, ndilija malo la pachogolo pa chamba idakwama paja ndi siidakoze kuchoka nampho pamalo papa chegela pa chamba padayamba kuduka kwa chifukwa ya ukali wa mafunde. 42 Mpango wa anyiwanja asikari odali ndi kwaapa omangidwa ili kuti palibe ambayo wadaka sambilila ndi kuthawa. 43 Nampho yujha askari wa jeshi la kiroma wadafuna kumlamicha Paulo mchimwecho wadauimika mpango wao, ndi wadalamula anyiwaja ambao akoza kusambilila, arumphe kuchoka mchamba huti ndia apite kumtunda. 44 Ndeyapo wachimuna wina siachate, wina pamwamba pa vipande va vitambwa ndi wina pamwamba pa vinthu vinancho kuchoka kuchamba kwa njila ii idachokela kuti enche sitifike.

Chapter 28

1 Yapo tidaikizidwa bwino tidajiwa kuti chilundwa Malta. 2 Wanthu apajua osati kuti adatila ndika bwinope, ikapanda adasonkha moto ndikutanila taonche ndandi ya vula ndi kuzizila uko kudalipo. 3 Nampho Paulo yapo wadasonkhanicha mtoro wa nkhani ndikuikha pachoso njoka yaing'ono ya malovu yoipa wadatuluka mumtoto mujha ndandi ya kuunola, ndikujivilinga pajanjha lake. 4 Waithu apajha yapo adaonanjokaijha indene kwa achinawene, munthu uyu ndi wakupha watawa kunyanja yamchele napho siwafunikukha wa moyo.'' 5 Nampho uje nyoka ijha wadaiponyo pachoso ndisiwadapwetikedwe. 6 Anyaio adamlindililia tuphi lake litupe kapina wagwe mwazizi ndikukumwalila. Nampho yapo amaphenya pa nyengo ya utali ndi kuona kuti palibe chinthu chadabwicha kwaiye adasintha maganizo yao ndi kunena kuti wadali Mulungu. 7 Pamalo paja pafupi padali nunda uo udali wamkulu wa chiumba munthu uyo wamatanidwa Pablio. Wadatilanila ndi kutisamala masiku yatatu. 8 Idaoneka kuti atati wake a Pablio adagwilidwa ndi malungo ndi kupesa ndi Paulo wadapitila, wadaphimpha ndi kuwa akila manja ndi kuwalamicha. 9 Baada ya lijha kutokea wandhu wina paja pachisiwani wajawadali wadwala pia wadapita ni kuwaponya. 10 Wanthu adatilimkeza ulemu wambili. Yapo timajikonja kunyamuka adatipacha timavifuna. 11 Pambuyo pa miyezi itatu tidanyamuka pachombo, cha Iskanda iyo imapepheteledwa ndi kuziziia pa chilumbapo, ndi achogoleli wake adali mabali amawila. 12 Pokafika kumujhi wa Sirakusa, tidakala pajha masiku ya tatu. 13 Kuchoka pajha tidanyamuka mbakana kukafika mujhi wa Regio, pambuyo pa masiku chimojhi mphempho ya kumwela inaonekana mwazizi, ndi pambuyo pamasiku yawili tidalowa mmujhi wa Putoli. 14 Kumeneko tidaakomana mabale akumojhi ndi adatilanda kukula nao masiku ya sano ndi yawili. Njiia imweyo tidaika ku Rumi. 15 Kuchoka kujha mabale anyiwajha, yapo adavela nkhani zatu, adajha kutilandi la kumsika wa Apias ndi nyumba za alendo zitatu. Yapo wadamuyamika Mulungu ndi kulimba mtima. 16 Yapo tidalowa Kuroma, Paulo wadaloledwa kukhala youha pamojhi ndi yiyha msikari wamamsunga. 17 Idadi pambuyo pa masiku ya tatu Paulo wadaatana pamojhi anyiwaja wachimuna adali achogoleli pakati pa Ayaudi. Yapo adasonkhanika waadakambila, achabale pamojhi kuti sinididalalakwe chilichonche kwa muthu anjawa kapina kulakwila mwambo wa achambu yatu atichogolela, ndindachochedwa ngati mkaidi kuchokela Kuyerusalemu mbakana mmanja ya Aroma. 18 Akate kundiuncha adakumbila kundimasula chifukwa padlije ndanda yofunika ine kuti ndi pendwe. 19 Nampho anyiwajha Ayahudi adakana, ndidakanamizidwa kuti mlandu wanga ndigwadile kwa Mfumu Kaisari ingakhale kuti sindimapeleko mlandu ku mtundu wanga. 20 Ndande yogwadila mumu, ndikupemphani kuonani ndi kukamba namwe, ndande kuti Islael achiyekezela, ndamangidwa ndi chingwe ichi. 21 Adamkambila, "sitidalandilepo karata kuchokela Kuyuda yokukhuza iwe. 22 Nampho tifuna kukuvela uganiza chiyani pakati pa gulu ili la wanthu yawa, chifukwa chake iwikana kwatu kuti tichuchana nao malo yaliyonche." 23 Yapo adapangana naye sikulu, wanthu ambili kupunda adaja yapo wamakhala wadaakambila ijha nkhani ndi kutilila umboni Ufumu wa Mulungu, wadayesa kwakokha kwa Yesu, kwa mtundu kawili kuchokela mmalamulo ya alosi kuyamba umawa mbakana ujhulo. 24 Akumojhi adaguzika pakati pa mauya jha yamakambidwa, nyengo wina sadakulupalile. 25 Yapo adalepela kuvana achinawene kwa achinawene, adachoka pambuyo pa Paulo kukamba mau limoji Mzimu Oyera udakamba bwino kupitila Isaya mlosi wacha atate wanu. 26 Wadakamba, pita kwa wanthu anyiyawa ukambe, mmakutu yanu simvele nanipho simvananavo, ndi kwa maso yano simuona nampho simjhiwa. 27 Ndande mitima ya wanthu anyiyawa yakala youma,makutu yao yavela kwa vutomaso yao atimila, kuti asajha kujiwa kwa maso yao, ndi kuvela mmakutu yao, ndi kuvana navo mmitima yao, ndi kung'ana mukancho, ndikuti ndidaka alamicha.'' 28 Kwaicho mfunika kujiwa kuti Mulungu watumiza chipuluso chake kwa wanthu a mitundu, ndi savechele, (penyelela mzeleku. 29 Nyengo wamakamba izi, Ayahudi adachoka, uku aliovutanavutana achinawene). 30 Paulo wadakala mnyumba yake yalendo panthawi ya viaka vuwili, ndi kulandila onche anyiyao adapita kwaiye. 31 Wamalalikila ufumu wa mlungu ndi kuyaluza vinthu pakati pa yesu Kristo pa mphamivu zonche ndi padalije wadamchekeleza.