Mwera: Bible for 1 Corinthians, 1 John, 1 Peter, 1 Thessalonians, 1 Timothy, 2 Corinthians, 2 John, 2 Peter, 2 Thessalonians, 2 Timothy, 3 John, Acts, Colossians, Ephesians, Galatians, Hebrews, James, John, Jude, Luke, Mark, Matthew, Philemon, Philippians, Revelation, Romans, Titus

Formatted for Translators

©2022 Wycliffe Associates
Released under a Creative Commons Attribution-ShareAlike 4.0 International License.
Bible Text: The English Unlocked Literal Bible (ULB)
©2017 Wycliffe Associates
Available at https://bibleineverylanguage.org/translations
The English Unlocked Literal Bible is based on the unfoldingWord® Literal Text, CC BY-SA 4.0. The original work of the unfoldingWord® Literal Text is available at https://unfoldingword.bible/ult/.
The ULB is licensed under the Creative Commons Attribution-ShareAlike 4.0 International License.
Notes: English ULB Translation Notes
©2017 Wycliffe Associates
Available at https://bibleineverylanguage.org/translations
The English ULB Translation Notes is based on the unfoldingWord translationNotes, under CC BY-SA 4.0. The original unfoldingWord work is available at https://unfoldingword.bible/utn.
The ULB Notes is licensed under the Creative Commons Attribution-ShareAlike 4.0 International License.
To view a copy of the CC BY-SA 4.0 license visit http://creativecommons.org/licenses/by-sa/4.0/
Below is a human-readable summary of (and not a substitute for) the license.
You are free to:
The licensor cannot revoke these freedoms as long as you follow the license terms.
Under the following conditions:
Notices:
You do not have to comply with the license for elements of the material in the public domain or where your use is permitted by an applicable exception or limitation.
No warranties are given. The license may not give you all of the permissions necessary for your intended use. For example, other rights such as publicity, privacy, or moral rights may limit how you use the material.

Matthew

Chapter 1

1Chitabu chakolo la Yesu Kristo mwana wa Daudi, mwana wa Ibrahimu. 2Ibrahimu wadali utate Aisaka, ndi Isaka atate Wayakobo, Ndiyakobo atate Ayuda ndi abale zake. 3Yuda wadali atate Apelesi ndi sela kwa tamali, Pelesi atate Wahezeloni, ndi Hezeloni atate Alamu.4Lamu wadali atate waAminadabu, Aminadabu atate Anashoni, Ndi Anashoni atate wa Asalimoni. 5Salimoni wadali atate Aboazi kwa Lahabu, Boazi atate Aobedi kwa Luth, Obedi atate Ayese, 6Yese wadali atate wa shifu wa Daudi. Daudi wadaliatate Asulemani kwa wakazi wa Uliya.7Sulemani wadali atate a Rehoboamu, Rehoboamu atate wa Abiya, Abiya atate Waasa. 8Asa wadali atate wake wa Yehoshafati atate wa Yoramu, ndi Yoramu atate a Uzia.9Uzia wadali atate a Yothamu, Yothamu atate a Ahazi, Ahazi atate a Hezekia. 10Hezekia wadali atate Manase, Manase atate a Amoi ndi Amoni atate a Yosia. 11Yosia wadali atate a Yekonia ndi kaka zake ndawi yotengedwa kupita kubali.12Ndi yake ndi Zerubabeli ndi pambuyo pauja usamicho wa Babeli Yekonia wa da mbala Shealtiel, Shealtiel wa da mbala Zerubabeli. 13Zerubabeli wadali atate a Abiudi, Abiudi atate a Eliakimu, na Eliakimu atate a Azori. 14Azori wadali atate a Zadoki, Zadoki atate a Akimu, ndi Akimu atate a Eliudi.15Eliudi wadali atate a Elieza, Elieza atate a Matani ndi Matani atate a Yakobo. 16Yakobo wadali atate a Yusufu munake Maliamu, ndekuti kwaniye Yesu wadabadwa, watanidwa Kristo. 17Vibadwa vonje tangu Ibrahimu mbaka Daudi vidali vibadwa kui ndi vinai, kuchoka Daudi hadi kutengedwa kupita Kubabebli hadi Kristo vibadwa kumi ndi vinai.18Kubadwa kwa Yesu Kristo kudali kwa mtu nduu amai wake, Maliamu, adachumbidwa ndi Yusufu, nambo pambuyo sadapezane, wadaonekana kukala ndimimba pa uwezo wa Mzimu Oyela. 19Mmunake Yusufu, wadali mundu uyo wali ndi ulemu siwadafune kumfezeesha pawandu wadamuwa kusiya ukwati wke pa siri.20Yapo wadali niwanganiza juu ya vindu ivo, angelo w ambuye wada mfikila pa ndoto, wadakama, "Yusufu mwana wa Daudi, usidaopa kumtenga Maliamu ngati mkazako, pandande mimba walinayo ndi kwa mbavu ya Mzimu Oyela. 21Siwajimasule mwana wa muna ndi siutane jina lake Yesu, pandande siwalamiche wandu wake ndi machimo yao."22Yonje yaya yadachitika kutimiza chija chidakambidwa ndi ambuye pa njila ya mlosi, adakama, 23"penya, bikira siwatenge mimba ndikubala mwana wa mmuna ndi samtane jina lake Imanueli," maana yake, "Mulungu pamoji nafe."24Yusufu wadauka kuchoka mulitulo ndi kuchi ngati angelo wa ambuye umoadakambila ndi wadamtenga ngati mkazake. 25Hata chocho, siwadagone nae mbaka yapo wadabala mwana wamuna ndi adamtana jna lake Yesu.

Chapter 2

1Pambuyo pa Yesu kubadwa pakati pa Bethelehemu pa Uyahudi pakati pa ufulu wa Helode wantu osoma kuchokela melo ya kutali adefika Kuyelusalemu ndiakamba, 2"walikuti mmeneyo wabadwa wali fulu wa Wayahudi? Tudaiona ntondwa yake kutali na fecho tabwela kumsulila." 3Pambuyo pavela yameneyo fulu Helode wa daipilwa ndi Yerusalemu yonche pamoji ndisye.4Helode wade alolika mapadre oche ndiokamba wawatu na yenche wade afucho Kristo siwa badwile kuti? 5Ada mkomejile "pakati pa Bethelehemu ya Ayahudi chifuko ndimo idolembedwale ndi oleta. 6Nawe Bethelehemu mujilo la ayahwelisiwa mngono pakati pa wakuru akuru ayude chifuko kuchokela kwaiwe siwajhe mchoroleli siwa asunge waufu wanga Izraeli."7Mvweno Helode adawa tena anyiwaja osome kwa pampepete wade afu cha ntawi yanji ntondwa ide onekana? 8Wade afuma Bethelehemu ndiwakema "mapotato kwa kujipenyelela mka mfunefune mwana wabadwa pa mene sompele mdeni palekele nkani zake dela kuti ine nonecho nikoze kuja kumabudu."9Pambuyo pakumvechela fulu Helode ade ade andekele ndi ulendo wao ndi utondwa iji adaisoe cho kupepete kwa jio idaeho getelo mpako yapo idoime pamalo ya mene mwana wabadwa wade tipo. 10Yapo adoiine ntondwa adefunge lalo kupunde.11Adeluwa munyumba ndikumwone mwana wa dodebadwa ndi Meliamo maiwake ade msalile ndi kumpembele ade mesolevuwene adetenga ndi kumchochela mwana mpoto yoninkira. 12Murungu wade akaniza, pamaluso kuti hade bwolelancho njila imeneyo achokela kwa Helode kwa muvemo ada bwela kuputa kujiko lao kupitila njila ino.13Pambuyo akungochoka kwao moraika ya Mulngu adechokela Yusufu pakati marufu nduku mkambile kuti Helode wa umfune funewana kuti wampe. 14Usiku umveo Yusufu wade uke ndiku mtenga ndi make ndi kutawila ku Misiri. 15Adekela kumeneko mpaka Herode yapo wade mwalile. Ichi chida chitiko kupitila chimene Mulungu wadechikombe kupitila orota kuchokela Kumisiri ne mtane mwa newanga.16Pambuyo Herode yapo wadeone anchita chipongwe ndi wantu ejwa wade kwiya kupunda wade peleka lamulo kuti waneonche waechimune ali Mbethelehemo ndionche meloyaya ache meneo alindi vyako viwili pachi kupambane ndintawi imeneyo wa deijiwa kuchokela kwa wantu waja osome.17Noteyapo lilevekela moulija lidedokela mkemwa mwa olota Yeremia. 18Sauti ida vekela moramehe malilo ndi metondo ulu ya akulu kupunda, Raheli ndi walilile wana wake ndi kama chipembezo chifuko adelipa waencho.19Yapo wada mwalile Herode panyani maraika ya Murungu wade mchokela Yusufu pamelosu Kumisiri ndikukenga. 20Ima umtenge mwane ndimake ndi mjopita kujiko le Isiraeli chifukwa ameneo amafuna kunja atokumwalile. 21Yusuphu wado imo kumtenga mwana ndimake ndi kufika jiko la iziraeli.22Nampo yapo wadevela kuti Arkelau ndiye wa imilila jiko la Yude pambuyo patate wake Herode wade epa kupwaje kupite kumeneko pambuyo pa Mulungu kuwa kanize pakati pa maloto wade choke ndikupita melo ya Ghalilaya. 23Ndwadepita kukale kumuji utimidwa Nazaleti chiimililidwe chide kambidwa panjira ya alosa kuti siwatanidwe Mnazareti.

Chapter 3

1Pa masiku yajhe Yohana mbatizaji waadaje kuilalikila pa pululu la Yuda ndikukambe. 2Lapani pakuti Ufumu wa kumwamba wawandikila. 3"Pakuti uyu ndiye wada nenedwa ndi olosa Isaya kunena mau ya mundhu watana kuchoka kupululu ikilantuni njila ya Ambuye, mongolani mwopita mwaiye."4Chipano Yoana wadavala maberega ya ngamia ndi lamba la chikwetu mchireno mwake. Chakudya chake chidali jhombe ndi uchi wa mtengo. 5Ndipo Yerusalemu Yuda yonche uzemgulila mchinje Yorodani kupita kwa iye. 6Adali kubatilizidwa ndiiye pa mchinje Yorodani ndi kulapa machimo yano.7Nampho yapo adaona ambili a mafarisayo ndi masadukayo ndi ajha kwa iye kubatizidwa adakambila anyiimwe vibadwa va njoka vitindisumu, yani uyo wakuofyani kuitawa mphwayi ito ikujha? 8Balani vipacho ino vifuna kulapa. 9Ndi msaalaganizila ndi kukambichana mkati mwanu. Tilinaye Ibrahimu ngati Mulungu wakoza kumkwezela Ibrahimu wana ingakale kuchoka kumyala yaya.10Tayari nkhwangwa yatoikidwa pa muzo wa mtengo. Ka icho kila mtengo osabele vipacho. Vabwino kudulidwa ndi kutaidwa kumoto. 11Ndi kubatizani kwa majhi kwa ndande ya chilapilo. Namphoiye wakuha pa mbuyo panga ndi wamkulu kupunda ine ndiine sinifunika kutenga vilato vake iye siwabatize kwa mzimu oyela ndi kwa moto. 12Ndi likelo lake lii mmanja mwaiye kuchuka nditu liwala lake ndi kuika pamojhi ngano yake mghokwe. Nampho siwabuche nkhupete kwa moto uwo siukoze kutimika.13Ndipo Yesu wadaje kuchoka Kugalilaya mpakana mchinje Yorodani kubatizidwa ndi Yohana. 14Nampho Yohana wadafuna kumchekeleza kukamba, "ine ndifuna kubatizidwa ndi iwe, ndi iwe ukujha kwa ine?" 15Yesu wadayankha kukamba, "vomeleza ikale chipano, pakuti ndi umoifunikila kukwanilicha malinga yonche." Ndipo Yohana wadavomela.16Pambuyo pa kubatizidwa pamwepo Yesu wadachoka pa majhi ndi penyani kumwambe kudamasaka kwa iye. Ndi wadamwona mzimu wa Mulungu wachika kwa chifanifani cha nkhunda ndi kudikila pa mwamba pake. 17Penyani mau lichoka kumwamba likamba, "uyu ni mwana wanga nimkonda. Ndikondendwe kupunda nndiiye."

Chapter 4

1Ndipo Yesu adachongozedwa ndi mzimu mbaka kupuluu kuti ayasedwe ndi Satana, 2yapo wadakala popanda kudya masiku makumi yanai. Usana ndi usiku, wadajivela njala. 3Oyesasa wadaja ndi kumkambila, "ngati ie mwana wa Mlungu kumula myalai ikale mkate." 4Nampho Yesu wadamuyankhandi kumkambila, "yalembedwa munthu siwakala kwa mkate oka nampho kwa mau lichoka mkamwa mwa Mlungu"5Ndipo satana wadampeleka kumuji woyela ndi kumuika pamwaqmba pa hekalu, 6ndi kumkambila, "ngati iwe mwana wa Mlungu, jiponye panchi, pakuti yalembedwa saalamula anjelo wake aje akutenge ndi kukunyakula kwa manja yao, kuti usajikuwala mwendo wako pamwala."7Yesu wadamkambila 'yalembedwacho' usamuyesa ambuye Mlungu wako. 8Ndipo satana wadamtenga ndi kumpeleka pamalo palipamwamba ndi kumlangiza zoko ndwelecho zonche za mjiko. 9Ndi kumkambila "sini kupache voncheri ngati ukanitamanda ndi kumilambia."10Ndip Yesu wadamkambila "pita uko uchoke pano satana pakuti yalembedwa ifunika umlambile ambuye Ambuye Mlungu wako ndi kumchitila utumiki iye yoka, 11"ndipo satana wadamsiya ndipo anjelo adaja kumchitila utumike.12Yesu yapo wadavela kuti Yohana wagwiidwa, wadachoka mbaku Kugalilaya. 13Wadachoka Kunazareti kupita kukala Kukapernaumu, ni mbali ya nyanja ya ya Galilaya, mmalie ya chigao cha Zabuloni ndi Naftali.14ichi chidachokela kumwanilicha chidakambidwa ndi Isaya olosa. 15Mmiji ya Zabuloni ndi Naftali kpita mnyanja, mchi dya ya Yordani, Galilaya ya wanthu osamjiwa Mlungu. 16Wanthu amakala kumdima aona dangalila lalikulu, ndi yao amakala mmalo mwa mtu nchi wa mjifa dangalila laawalila.17Yengo imeneyo Yesu wadayamba kulalika ndi kukamba, "Lapani pakuti ufumu wa kumwamba wawandikila,"18yapo wamaenda mbali ya myanja ya Galilaya wadaaona abale awili, Simoni watanidwa Petro ndi Andrea m'bale wake nda chela makoka mnyanja pakuti adali ovua nchomba. 19Yesu wadaakambila, majani nichateni, sinikuchiteni ovula wanthu. 20Maraka moji adayasiya makoka ndi kumchata.21Yesu yapo wadaendekela kuchoka paja wadaao na abale wina awili Yakobo mwana wa Zebedayo ndi Yohana m'bale wake. Adali m'bwato ndi Zebedayo tate wao amasoka makoka yao wadaatana. 22Mara kamoji adasiya bwato ndi atate wao ndi kumchata.23Yeu wadayenda Mgalilaya yonche,ndi kuyaluza mmasinagogi yao kulalika utenga wa Ufumu, ndi kuchilisa nthenda za mitundu mitundu mwatimwao. 24Nkhani zake zidaenela Siria yonche, wanthu adapeleka wanthu onche yao amavutika, ndi matenda namtundu mtundu, ndi kupweteka adali ndi mizimu yoipa anjilinjilindi opoloza Yesu wadaachilisa, 25gulu la wanthu lidamchata kuchoka Kugalilaya, ndi Dekapoli, ndi Yerusalemu ndi kwa Ayuda ndi kuchokala kuchidya ya Yordani.

Chapter 5

1Yesu yapowadauona mtiti, wadachoka ndi kupta kuphili, yapo wadakala panchi,opuzila adajha kwa iye. 2Wadamasula pakamwa pake ndi kuwayaluza, wadakamba. 3Mbasa anyiyao ali amphawi amzimu, chifuko ufumu wa kumwamba ndi wao. 4Mbasa anyiyao ali ndi chisoni, chifuko sathondozedwe.5Mbasa anyiyao ali ojichicha, chifuka saasidwile jhiko. 6Mbasa anyiyao ali ndi njala ndi lujho la chazene, chifuo anyaiwo sakhutichidwe. 7Mbasa anyiyao alekelela, chifuko nao salekeledwe. 8Mbasa anyiyao ali ndi mtima oela, chifuko samuone Mulungu.9Mbasa anyiyao avanichana, chifuko anyaio saatanidwe wana Amulungu. 10Mbasa anyiyao azunjika kwa chifuko chazene, chifuko ufumu wa kumwamba ni wao.11Mbasa anyiyao wathu sakutukwani ndi kuuzunjani, kapena kukukambani kila mtundu oipa pakati panu kwa unami kwa chifuko changa. 12Kondwani ndi kululutila, ndande mphoto yanu ni yaikulu kumwamba, pakuti nde n'chimwecho wantu umowaazunjila alosa anyiyao adalipo kabla ya anyaimwe.13Anyaimwe ni n'chele wa jhiko. Nampho ngati n'chele wasoweza kakomedwe kake, siikezencho bwanji kukhala n'chelencho? Notho siukoza kukala wa bwino kwa chinthu chalichonchecho ingakale ni kutaidwa kubwalo ndi kupondedwa ndi myendo ya wanthu. 14Anyaimwe ni dangatila la jhiko mujhi uo wamangidwa paphili siubisika.15Wala wanthu sakweleza nyali ndi kuiika panchi pa mswche, nampho poonekela nayo yamulika onche anyiyo ali mkati mwa nyumba. 16Siya dangatila lanu liwale pamaso pawanthu pakuti ayione vichito vake va bwino ndi akuzike atate wanu ali kumwamba.17Msadaganiila najha kuliwananga lamul kapena olosa. Sinidajhe kuwananga nampho kulikwanicha. 18Kwa chazene nikukambilani kuti kumwamba ndi jhiko vonche vipite palibe yodi imojhi kapena nukta imojhi ya tauko silichochedwe pakati pa tauko mbaka yapo kila chinthu yapo sichikale chata kuenela.19Kwaicho waliyonche uyo siwatyole lamulo laling'ono limojhi ndi kuwayaluza wina kuchita nchimwecho siwatanidwe wamng'ono pakati pa ufumu wa kumwamba. Nampho walionche wayagwila ndi kuyayaluza siwatanidwe wamkulu pakati pa ufumu wa kumwamba. 20Kwa mate nikukambilani haki yanu ikasiya kuchuluka haki ya olemba ndi afarisayo, kwa valiyonche vijha simulowa ufumu wa kumwamba.21Mwavela adakambidwa kale kuti, "usadapha" ndi valiyonche wakupha wali pakati pa kuluswa kwa chilango. 22Nampho nikukambilani walyonche wamuipia m'bale wake siwakale pakati pakiluswa kwa chilango. Ndi waliyonche wamkambila m'bale kuti, "iwe ni munthu uyo siukwanila!" Siwakale pakati pa bwalo la kuluswa.23Kwaicho ngati uchocha nchembe yako pakati pa mazabao ndi ukumbukila kuti m'bale wako wali ndi chinthu chalichonche pakati pako, 24isiye nchembe yako pakati pa mazabau, kwaicho gwila njila yako. Kavanichaneni payamba ndi m'bale wako, ndipo ubwele uchoche nchembe yako.25Mvanichane ndi olakwa wako chisanga, ukakhala pamoji nae mnjila popita kuboma, mwina mwake olakwa wako wakoza kukusiya mmanja mwa hakimu ndi hakimu kukusiya mmanja mwa askri ndi iwe kusiidwa m'boma. 26Muamini nikukambilani, notho siusiidwa uhulu hadi ulipe senti yotela iyo umadaidwa.27Navela yakambidwa kuti, "msadachita chitole." 28Nampho nikukambilani waliyonche wambenya wamkazi kwa kumkhumbila wathochita nae chitole mumtima mwake.29Ni nati diso laku la kwene lchiticha kujikuwala, lizule ndi ulitae kwa kutali nawe. Ndi pakuti mbasa chiwalo chako chimoji pathupi lako chiwanangike kuliko thupi la mphu mphu litaidwe kujhehanam. 30Ndi ngati jhanja lako la kwene lichiticha kujhikuwala, lidude ndi ulitae kwa kutali ndi iwe. Pakuti mbasa chiwalo chimojhi patupi lako chiwanangike kuliko thupi la mphu mphu litaidwe kujhehanam.31Yakamidwa kuti waliyonche wampopola mkazake wampache malembo ya milandu. 32Nampho ine nikukambilani, waliyonche wa msiya mkazake, ingakale kwa ndande ya chitole, wamchita kuti wachidekete. Ndi waliyonche uyo siwamkwatile pambuyo pakupachidwa malembo ya milandu siwachite chidekete.33Nampho mudavela idakambidwa, kwa anyiwajha akale, msadalumbila kwa unami nampho vipelekeni vilanga vanu kwa Mulungu. 34Nampho nikukambilani, msadalumbila ata pang'ono kapena kumwamba ndande nyengo ya mulungu. Kapena kumwamba ndande nyengo ya mulungu. 35Kapena kwa jhiko, mate yake ni pamalo poika mpando opondela mapazi yake, kapena kwa Jhelusalemu, pakuti ni mujhi wa mfumu wa mkulu.36Ata usadalumbila kwa mutu wako, mate yake siukoza kulichita chichi limojhi kukhala loela kapena lakuda. 37Chipano mau yanu yakale, "nchimwecho, chimwecho, opande, opande" pakuti yapundayo yayo yachoka kwa yujha olakwa.38Mwavela yakambidwa kuti, "diso kwa diso, ndi jhino kwa jhino." 39Nampho ine nimambila, msadashindana kwa olakwa, nampho munthu wakakubula chakaya la kwene mng'anamulile ndi linjakencho.40Ndi waliyonche wakulamua kupita nae maili imojhi pita nae maili ziwili. 41Kwa waliyonche wakupempha mpache, ndi usadam'basala waliyonche uyo wfuna kukukongola. 42Ndi ngati waliyonche wakumbila kupita ndi iwe kuboma ndi kukulanda kanzu lako, msiile ndi jhoho lako!43Mwavela yakambidwa, "umkonde wapafupi wako ndi umuipile mdani wako!" 44Nampho nikukambilani, "akondeni adani wanu, apempheleni anyiyao akudandaulichani, 45Nampho kuti mukale wana wa atate wanu ali kumwamba. Pakuti alichita jhuwa lawalile oipa ndi abwino, ndi akunyechelani vula olakwa ndi abwino."46Ngati simwakonde anyiyao akukondani anyaime, mupata yanji. 47Ningati mukaalonjela achaabale wanupe mupata chiyani kwaapitilila wina? Bwanji wantu ammaiko sachita nchimwecho? 48Kwa chimwecho itifuna kukala okwanila, ngati atate wanu akumwamba umoali okwanila.

Chapter 6

1Zingatila kutokuchita vintu vabwino mbeleza wantu ili kujilangiza, mwinamwake si upata ulemelelo kuchoka kwa ambuye alikumwamba. 2Kwachimwecho basi yapotichocha siudatimba tarumbeta ndi kujisifu umwene ngati wanafiki umoachitila katika makanisa ndikatika mitaa ili uti wantu atukuze. Kweli nikukambilani, atolandila thawabu yao.3Nampho iwe yapouchocha janjalako lakushoto silidajiwa ichochichitika ndijanja lakumanjele. 4Ili kuti mphaso yako ichonchedwe kwa siri. Ndiyapo ambuye wako apenya sirini siakuache thawabu yako.5Ndiyapo upempha, siudkala ngati mnafiki, pakuti akonda kuima ndikupempha makanisa ndi mkona za mmitaa, ili kuti wantu apenye. Kweli nikukambilani atolandila thawabu yao. 6Nampho iwe, yapoupemba, lowa kuchumba, cheka chicheko ndi upemphe kwa ambuye wako alikobisika, ndeambuye wako yaoapenya kabisika ndipo ambuye wako apenyako bisika siakupache thawabu yako. 7Ndiyapo upempha, siumabwelela mau yalibe ndi maana ngati mataifa umoachitika pakuti wanafiki kuti savele kwachifuko chamau yambili yayoayakamba.8Kwachimwecho, siudakala ngati anyioo, pakuti ambuye wao wajiwa mahitaji yao ata kabla siudapemphe kwake. 9Chimwecho basi pemphani chimwe, Ambuye wantu ulikumwama, litukuze jina lako. 10Uflume wako uje, mapenzi yako yakwanize pano pajiko ngati kumeko kumwamba.11Utupache mkate watu wa kila nyengo. 12Utidalise adeni, ngati ife muja taalekelela wadeni watu. 13Ndi siudatipeleka kupila mayeso, nampho utuepushe kuchokela kwa yuja oipa.14Ikakala simwalekelela volakwa vao wala ambuye wanu siakulekelelani volakwa vanu. 15Nampho ikakala simwalekelela volakwa vao wala ambuye siakulekeleni anyiimwe.16Zaidi ya yonche yapoukala wamanga, siudalangiza sura yachisoni ngati wanafiki mujaachitila pakuti akwinya nkhope zao ili kuti wantu ajiwe amanga, kweli nikukambilani atokala kulandila thawbu ya. 17Nampho iwe, yapoukala wa manga, paka mafuta mmutu mwako ndi uchuke kumaso kwako. 18Chimwecho siukulangiza panchogolo pa wantu kuti wamanga, nampho tusiikale kwa ambuye wako alikobisika. Ndi aambuye wako uyowaona kobisika, siakupacheni mphaso yanu.19Siudajikila chintu yako umwene pano pajiko, ambapo nondo ndi kutu siwakza tyola ndi kuba. 20Pambuyo pake, jiikile chintu yako umwene kumwamba ambapo wala nondo wakutu siikoza kuwananga ndi ambapo ankungu siakoza kutyola ndikuba. 21Pakuti chintu yako ilipo, nde yapo mtima wako yaposikalepo.22Diso ndi taa ya mtupi. Kwa chimwecho, ikakala diso lako ndi zima, tupi lonche siilendi mwanga. 23Nampho ikakala diso lako ndi lowanangika, mtupi mwako monche mwajala mdima totoro. Kwachimwecho, ikakala dangalila ambalo lilimo mkati mwako ndi mdima waukulu kiasi chanji! 24Palibe hata mmoji uyowakoza kuwatumikila achaambuye awili, pakuti siwamuipile mmoji ndi kumkonda mwina au lasivyo siwajichoche kwammoji ndi kumdharau mwina. Simkoza kwatumiilaa Mulungu ndi chuma.25Kwachimwecho nikukambila, usidakala ndi manta kuhusu maisha yako, kuti siudye chiyani au siumwe chiyani au kuhusu tupi lako, siuvale chiyani bwa maisha yako si zaidi ya vakudya ndi tupi zaidi ya vovala. 26Penyani mbalame alikumwamba, siavyata ndi siavuma ndi sakusanya ndikusunga mghala, nampho ambuye wanu akumwamba ajecha anyiio, bwa anyiimwe si athamani zadi kuliko anyio.27Ndiyani kati yanu kwa kujihangaisha wakoza kuongeza ridha imoji kuumoyo wa malamidwe yake. 28Ndindande yanji mkala ndi mantamanta kupitila vivalo gani zilanikhusu madua mmunda, jinsi umo yakalila. Siyachitanchito ndisi yakoza kujiveka. 29Nikali kukukambilani, hata Sulemani atika utukufu wake onche siwadavekedwe ngati mmoji wao wayaya.30Ikakala Mulungu wayavalicha machamba katika mmunda, ambapo yadum siku limoji ndi mawa yataidwa katika moto, bwa nikwantawi yanji siavaliche imwe. Imwe machinawene imani yaing'ono. 31Kwa chimwecho simdakala ndi manta manta ndikukamba, bwa sitidye chiyani? Au bwa sitimwe chiyani? Au bwa sitivale nchalu zanji,.32Pakuti mataifa afunafuna vintu ivi, ndi ambuye wanu akumwamba wajiwakuti muyafuna yamene. 33Nampho kwaza funafunani uflume wake ndi haki yake ndi yaya yonche siyakabizidwe kwao. 34Kwa chimwecho siudaona manta kwaajili yamawa pakuti mawa sijihangaikile ene, kila siku ikoza kukalandi vuto lake lene.

Chapter 7

1Usalamula, ni iwe usaja kulamlidwa. 2Kwa lamulo ulamula, ni iwe ulamulidwe. Ni kwachilino upimila ni iwe nawe upimilidwe chimwecho.3Ni kwandande yanji upenya chipand cha mtengo chili kudiso la mbale wako, nampho siujiwa chipande cha gogo icho chili katika diso lako? 4Ukoza bwanji kukamba kwa mbale wako, lindila nikuchochele chipande chili mdiso lako, wakati chipande cha gogo chili mkati mwa diso lako. 5Wamtila iwe: Poyamba choche gogo lili mdiso lako, nde yapo ukoze kupenya bwino ni kuchichoche chipande cha mtengo chilimo mdiso la m'bale wako.6Usapacha angalu chili choela, ni usaponyela nkhumba chakuja pachongolo pao. Vinginevyo saviwanange ni kuviponda kwa myendo, ni tena siakung'ana mukile iwe ni kukupweteka vipande vipande.7Pempha, nawe upate funa, nawe upate. Bisha hodi ni iwe umasulilidwe. 8Kwa waliyonche wapempha, walandila ni kwa waliyonche wafunafuna, wapata. Ni kwa munthu uyo wabisha hodi, wamasulidwila. 9Au kuli munthu kati yanu uyo, ikakala mwana wake wampempha chipande cha mkate wampache mwala? 10Au ikakala wampempha nehhomba, ni iye wampache njoka?11Kwa icho, ikakala anyiimwe muli oipa mjiwa kwapache achanawamu zawadi ya bwino, bwanji! Ni kiasi chanji zaidi apate ali kumwamba wakupacheni vinthu vabwino anyiaja ampempho iye? 12Kwa ndande imeneyo, yapo ufuna kuchitidwila chinthu chalichonche ni wanthu wina, nawe pia ifunika kwa chitila chimwecho anyiio. Pakuti limenelo ni lamulo ni mlose.13Lowami kupitila komo laling'ono, pakuti komo ni lalikulu ni njila ni yaitali ichongoze kupitta kowananga ni kuli ambili apita njila imeneyo. 14Njila ya ing'ono i njila ichongoze katika umoyo ni mochela akoza kuiona.15Jisungeni ni mlose au nami, akuja avala chikwtu cha mbelele, nampho uzene ni agalu ong'ang'ala. 16Kwa vichito vao mwajiwe, Bwanji wanthu akoze kuvuna matunda mminga, au mtini muli mbeu ya mibaruti? 17Kwa jinsi imeneyo, kila mtengo wa bwino ubala matunda ya bwino, nampho mtengo oipa ubala matendo yoipa.18Mtengo wa bwino siukoza kubala matunda yoipa, wala mtengo oipa kubala matunda ya bwino. 19Kila mtengo uo siubala matunda ya bwino udulidwe ni kutaidwa katika moto. 20Chimwecho basi, wajiwe kuchokana ni vichito vao.21Asati kila munthu wanikamila ine; Ambuye, Ambuye, walowe katika ufumu wa kumwamba ila ni yuja ambaye wachita vichito va atata wanga ali kumwamba. 22Wanthu ambili anikambile siku limenelo, Ambue, Ambuye, tida lose kwa jina lanu, tidachoche mizimu kwa jina lnu, ni kwa jina lanu tidachite vichito vambili vavikulu? 23Nde yapo nikukambilani padanga, sinikujwani anyiimwe! Chokani kwanga, anyiimwe chita woipa!24Kwa icho kila mmoji wavela mau yanga ni kujalemekeza walingane ni munthu wali ni njelu wamanga nyumba yake pamwamba pa pili. 25Vula idanya, mafuriko yadaja, ni mphepo idaja idabula nyumba imeneyo, nampho siidakze kugwa panchi, chifuko idali yamangidwa pamwamba pa pili.26Nampho kila munthu walivela mau langa ni siwali lemekeza, walinganichidwe ni munthu owewela wamanga nyumba yake pamwamba pa mchenga. 27Vula idaja, mafuriko yadaja, ni mphepo daja kuibula nyumba imeneyo. Ni idagwa, kuwanangika kwake kudakamilika.28Udafika muda ambao Mpulumusi wadamaliza kukamba mau yaya, wanthu adazichidwa ni mayaluzo yake. 29Pakuti wadayaluza ngati munthu wali ni cheo ni osati ngati otenga nkhani wao.

Chapter 8

1Nyengo Yesu yapodachika panchi kuchoka kupili, gulu la likulu lidamnchota. 2Penya, mkoma luadaja ndi kagwada pancho gola pake wadakamba, "Ambue, ikankala ulitayari, ukola kunichita ninkale bwino." 3Yesu wadanyosha nchancha lake ndi kumgusa, wadakamba, "nili tayari, ukale bwino." Pamwepo wadaela ukama wake.4Yesu wadamkambila, "penya kuti siudakamba kwa munthu waliyonche gwila nchila yako, ndi ujionyeshe umwene kwa wanchembe ndi uchache mphaso amayo Musa wadaagiza, kwa ndande ya ushuhuda kwao."5Nyengo Yesu yapo wadafika Kapernaumu, jemedari wadaja kwake wamfuncha. 6Wadakamba, "Ambuye, mtumiki wanga wagon kunkoma wa poozandiwali ndi kupwetekedwa kwa kuofya." 7Yesu wadamkambila, "sindije ndi kumlamicha."8Jemedari wadajibu ndi kumkambila, "Ambuye, ine osati wa mate ata uje ndi kulowa mkati ma nchancha langa, kamba maupe ndi mtumiki wanga siwalame." 9Pakuti ine nane ndi munthu ndili ndi malamulo, ndi nilinao askari ali wa panchi panga. Nikakamba uyu "pita ndi mwinancho manch na yo wakuncha, ndi kwa mtumiki wanga, chita mchimwechi ndi iye wachita mchi mwecho. 10Nyengo Yesu yapo wadavela yaya, wadadwaa ndi kwaakambia anyiwa ncha ama mchota "uzene ndi kukambilani, sinidapate kuona munthu mwene chinkulupi ngati uyu pakati pa Israeli."11Nikukambilani, ambili sianche kuchoka Mashariki ndi Magharibi, siankale pameza pamaji ndi Ibrahimu, Isaka, ndi Yakobo pakati pa uumu wa kumwamba. 12Nampho wana wa mfumu siataidwe mkati mwa mdima la kubwalo, ambaka sikunkaleka ndi chililo ndi kutafuna mano. 13Yesu wadamkambila jemadari, "mapita! Ngati umoji wantho kulupalila ndi ichitike mchimwecho," ndi mtumiki wadawadalamichidwa pakati pa saa iija.14Nyengo Yesu yapo wadafika pa kama pa Petro, wadamwona mpangozi wa wake Petro wagona wadwala homa. 15Yesu waamgusa nchancha lake, ndi homa yake idamsia. Nde yapo wadauka wadayamba kumtandiza.16Ndi yapoudafika ujulo, wanthu adampelekela Yesu ambili anyiyawo ada tawalidwa ni mizimu. Wadawatamangincha mizimu ndi anyiwancha amadwala wadalamincha. 17Kwa ndande ii yadotimizidwa yancha ya danta kukambidwa ndi Isaya olasa, "iye mwene wadatenga kudwala kwanthu ndi wadatenga vodwala vanthu."18ndeyapo Yesu wadaona gulu lamzungulila, wadachancha maelekezo ya kpita bendeka lina lanyancha ya Galilaya. 19Ndeyapo alemba wadancha kwake ndi kumkambila, "pulisi, sindikuchate paliponche yaposiupite." 20Yesu wadamkambila' "galu wamntengo wali ndi maenche, ndi mbalami wa kumwamba wilini chisa, pa kuganeka muntu wake."21Opuzila mwina wadamkambila, "mbuye, niruhusu huti nipite kumzika tate wanga." 22Nampho Yesu wadamkambila, "nichote, ndi uwasie akufa azikane kwa akufa wao."23Yesu yapowadalowa mkai mwa bwata, apuzila wake adamchota mbwata. 24Penya, yadainuka mafunde yaya kulu pa mwamba pa nyancha, kiasi cha bwato udabila ndi mafunde. Nampho Yesu wadagona. 25Opuzila adaja kwake ndi kumuncha adakamba, "Ambuye, mtuokoe ife, tuelekea kufa!"26Yesu wadaakambila, "ndande chiyani muapa, anyiimwe muli ndi chikulupi cha ching'ono? Ndeyapo wadauka ndi kukalipila mphepa ndi nyancha. Ndeyapo kudatulia sana, 27wachimuna adagwilidwa ndi kuduaa adakamba, "uyu ndi wamtundu wanchi, kuti ata mphepo ndi nyancha vimvenchela iye?"28Nyengo Yesu yapo wadaja bendeka lina la jhiko la magadala, wachimuna awili anyiyawoatawalidwa ndi mizimu adapezana naye. Amachokela kama kaburi ndi amachita vurugu sana iasi cha kuti palibe asafili wadakankoza kupita njila incha. 29Penya, adachoncha sauti ndi kukamba, "tulindichi yani cha kuchita kwako, mwana wa Mulung? Wada pana kututesa kabla ya nyengo kufika?"30Chipana gulu la likulu la nguluwe lidali niliwasa, sipadali papatali sana yapoadali. 31Mizimu adaendelea kulalamika kwa Yesu ndi kukamba, "ikankala siutu lamule kuchaka, tupeleke pa gulu la nguruwe." 32Yesu wadakambila, "pitani!" mizimu idichaandi kupita wa nguruwe, ndi penya, gulu lonche lidachika kucheka kupili kuchikilila kunyancha ndi lonche ldafila mmanchi.33Wachimuna amawesa nguruwe adantawa. Ndi yapo adapita kumjini adaeleza kila chinthu, hasa ichachidachokea kwa achimuna anyiwayawa ndi mizimu. 34Penya, mji mzima udaja kupezana ndi Yesu. Yapo adamwona, adapempha wachoke kupita mkea wao.

Chapter 9

1Yesu wadalowa mchombo ndi kuyomboka nyanja mbakana mujui uwo wamakhala. 2Onani, adamuphelekela mnthu onyongolola wagonekhedwa pa machira. Vaph wadaona chikulupi chao, Yesu wadamkhambila munthu anyongolokayo mwana wanga khala akondwa, machimo yako ya kulululikidwa.3Amphuzisi wina amalamulo adayamba kufunchana munthu uyu wachita chipongwe. 4Yesu wadajhiwa maganizo yao ndi kunena ndande chiyani mganiza kuipha mmitima wanu? 5Chamsanga kunena ndi chiti, wakululukidwa machimo yako kupima ima mapita. 6Nampho mjhiwe kuti mwana w munthu wali ndi mphamvu zokululukila machimo wadakama yaya kwayajha munthu onyongoloka, "ima tenga chogonela chako mapita kumujhi wako."7Munthu yujha wadaima ndikupita ku mujhi wake. 8Wanthu wonche yapoadaona adadabwa, ndi kuyamba kutamanda Mulungu, iye waapa cha wanthu mphamvu zimenezo. 9Yesu yapo wadachoka pajha wadamuona munthu amamtana Mathayo, wadakhala mbali ya osonkhecha sonkho. Iye wadambila ndichate ine, iye naye wadauma ndikumchatha.10Yesu yapho wadali mnyumba kuti wadye chakudya, adajha osonkhecha sonkho ambili ndiwanthu olakwa adadya chakudya pamoji ndi Yesu ndi omphuzira wake. 11Yapho adaona izi Afarisayo wadakambila omphuzila, ndande chiyani mphuzisi wanu wakudya chakudya ndi wanthu osonkhecha sonkho ndi wnthu amachimo?12Yesu yapho wadavela, naye wadakamba wantu yao alibwino sangafune sing'anga, ikapanda anyiwajha adwala. 13Mfunika mkajhiyaluze mate yake, ndikonda chifundo ndiosathi nchembe, pakuti sindidajhe kwa okhulupalila, ikapanda ndajha kwa ochimwa.14Ndip omphuzira a Yohana adamchatha Yesu ndikunena kuti ndande chiyani ife ndi Afarisayo timanga, nampho omphuzira wako samanga? 15Yesu wadayankha, bwanji ophelekeza ukwati akhoza kukhalandi chisoni nyengo mkhwatiyo alinayo pa mwepho? Nampho masiku yakubwela mkwatiyo kutengedwa kuchokela kwa anyaio, ndipo yapho samange.16Palijhe munthu waika nchalu za chiphano machalu za kale, chigamba siching'ambidwa kwake kukhala kwakukhulu.17Palijhe wanthu akhoza kutila vinyo ya chiphano mmatumba ya kale, ngati akachita chimwecho tumba siling'ambike, pambuyo pake vinyo yachipano ikidwa mtumba la chipano ndivonche vikhala bwino.18Nengo Yesu wamaakhambila mau yaya, wadajha wa mkhulu ndi kugwada pa maso pake, iye wadakamba, mana wanga wa mkazi wamwalila pafupi yapha, nampho majha lemuikhe jhanja walame. 19Yesu wadaima ndikumchata pamojhi ndiomphuzira wake.20Onani, wamkazi uyo wamatuluka nkhole pa nyengo ya viaka khumi ndi viwili, wadamsendelela Yesu, ndukugunda mponje wa chivalo chake. 21Pakuti wadamkamba ndikagunda mphonji wa chivalo chake sindisangalale. 22Yesu wadang'anamuka ndi kumphenya ndi kumkambila, mwali limba mtima chikulupi chako chakuchita usangalale, nyengo imweyo wamkazi wadalama.23Yapo wadalowa mnyumba ya wamkhulu Yesu, wadaaona wanthu atimba mbetete ndi gulu la wanthu amachita mapokoso. 24Iye wadaakambila, chokhani yapha, pakuti mwali siwadamwalize, ikapanda wagona. Nampho anyaio adasekaseka ndi kumnyodola.25Yapho adatuluchidwa kubwalo anyiwajha wanthu iye wadalowa kuchipinda ndi kumgwila janjha ndi yujha mwali wadauka. 26Ndi nkhani iyi idawanda mujhi wonche. .27Yesu yapowadachoka pajua wachimuna awili osapenye adamchotha. Ndikukweza mau kukhamba mwana wa Daudi utichitile chifundo. 28Nyengo Yesu wafika pa nyumba, anyiwaja osapenye adamchata, Yesu wadaakambila mkulupalila kuti ndi khoza kuchita? Nao adayankha yetu ambuye.29Yesu wadaagunda maso yao ndikunena ichitike chimwecho kwanu ngati hikulupi chanu umo chili. 30Maso yao yadamasukha, Yesu kwa mphamvu wadaalamula kuti asadamka mbila munthu waliyonche nkhani izi. 31Nampho awili aniwaja adachokha ndi kupita kulengeza mujhi wonche.32Wachimuna awili amaenda njila, onani, munthu mmojhi sakhamba wagwilida ndi mizimu yoipha wadapelekhedwa ka Yesu. 33Ndi mizimu yoipha idamchoka yujha munthu sakamba wadayamba kukhamba, gulu lidadabwa ndikukhama izi zidaonekepo Israeli yonche. 34Nampho Afarisayo amakamba, "mizimu yoipa yamatangichidwa kwa wamkhuli wa miziu yoipha."35Yesu wadapita mijhi ndi mizinda yonche. Iye wamapita kuyaluza mnyumba zao za maphemphelo, wamalalikila utenga wa ufumu, ndikulamicha matenda ya mtundumtundu ndi kufookwa kwa mtundu wonche. 36Yapo adaliona gulu, wadalilengela lisungu, ndande wadachauchika ndi kutyoka mtima adali ngati mbelele zilijhe owesa.37Yesu wadaakambila omphuzira wake, vinthu vachuluka, nampho anchito achepha. 38Kwaicho amphempheni ambuye apeleke wanthu anchito.

Chapter 10

1Yesu adawaitana opuzila wake kumi ndi awili pamoji kuti malamulo pamwamba viwanda vichafu, kuvikalipila ndi kuvitopola ndikulama aina zonje zamatenda ndi naina zonje zandenda.2Majina yatumiki kumi ndi awili ndi ya loyamba Simiyoni (ndiposo aitanidwa Petro), ndi Andreya kaka wake, Yakobo mwana wa Zebedayo, ndi Yohana kaka wake. 3Philipo, na Bertelemayo. Tomasi, ndi Matayo mtoza ushuru, Yakobo mwna wa Alfayo, ndi Tadeo, 4Simoni mkananayo, ndi Yuda Iskariote, uyo wadamgwilicha.5Yawa awili Yesu adatuma. Naye wadakambilila wadakamba, "msidapita pamalo uko ankala anjikho ndi simudalowa mmiji mwa Asamalia." 6Pambuyo pake, mpite kwa khosa izozasowa anyumba ya Israeli. 7Ndi yapompita, pembelani ndi kukamba, ufulu wa kumwamba wawandikila!8Lamichani odwala uchani akufa, lamichani amakate ndi topolani viwanda malandila chaje, chochani chanje. 9Msidatenga dhahabu, almasi au shaba mpochi zanu. 10Msidatenga mkoba paulendo wanu, kapena njalu za pambepete, vilatu pena chiboko, pakuti ndaka isitaili chakuja chake.11Muji walionje pena chijiji ichosimulowe, funafunani uyo wafaa ndi mkale pamenepo mbaka yapo simuchoke. 12Yapo simulowe mnyumba lonjelani, 13kapena nyumba iyo yafaa, amani yanu ikale paja, nambo ngati nyumba siifaa,amani yanu ichoke pamoji namwe.14Ndi kwa waja sakulandilani anyiimwe kapena kuvea mauyanu, ndawi ndi mchoka mnyuma au pamuji wo, jichanguleni malifumbi ya mapazi yanu pamalopo. 15Uzene nikukambilani, sikale yolama kupunda muji wa Sodoma ndi Gomola siku laukumu kuposa muji umene.16Penyani, nikutumani ngati mbelele pakati pakgalu atengo, kwaicho kalani okhaniza ngati njoka ndi zipole ngati ngunda. 17Mkale ajipenyelele ndiwanda, skupelekeni mndende, ndikuku menyani mnyumba. 18Ndi simupulekedwa pachongolo pawakulu ndi a chongoleli panande yanga, ngati uvome ulo wao ndi kwajiko.19Ndawi yaposaku shutumuni, msidakala ndi kuopa njilala yanji au chiyani cha khamba, pakuti chindu chokamba simuni ngindwe pandawi imweyo. 20Pakuti opande anyiimwe simkambe, nambo mzimu watate wanu sukambe mkati mwanu.21Mm'bale siwamukilele mm'bale wake kumpa, ndi tate kwa mwana wake, wana sauke dhidi yawana ndi kwafunila nyifa. 22Namwe simuipidwe ndikila mundu pa ndande yajina langu. Nambo walionje uyo sialimbe mbaka mmatelo mundu mmene siwaokoledwe. 23Ndawi iyo atesedwa pamuji umene. Tawilani pamuji uwo uchatila, pauzene nikuuzani simukala mapita mmiji yoje ya Israeli pambuyo pa mwana wa damu wakali osabwela.24Opuzila opande wamkulu kuposa mpuzisi wake, wala otumidwa wali pamwmba pa abwana wake. 25Ikwana kwa opuzila kuti wakale ngati opuzila wake.26Chochonbasi msidaopa anyiiwo, pakuti palibe ndindi icho sichimaulidwa, ndi palibe chabisika icho sichijiwikana. 27Icho nikukambilani mudima, mkakamba kwacha, ndi icho muchivela kwaa ulahisi mmasikiyo yanu, muhitangaze mkakala pamwamba pamwamba panyumba.28Msidaopa waja akupa tupi nambo alibe mbavu zakupa mzimu. Pambuyo pake muopeni yuja wakoza kupatupi ndi mzimu kuja kuzimu. 29Bwa kasuku awili sakgulichidwa pa mtengo waungono? Ata choho palibe wakoza kugwa pai bila atate wanu kujiwa. 30Nambo atachijiwicho cha machichi yanu cha yawelengedwa. 31Msidakala ndianda, pakati mtengo wanu waukulu kunda oposa kasuku ambili.32Chocho basi kila mmoji uyo siwanilisi pamaso pawandu, naneso sindimvomele pamaso paatate wanga akumwamba. 33Nambo uyo siwanikane pamaso pawandu, nane chocho sindimkane pamaso pautate wanga ali kumwamba.34Msidakhaniza kuti nabwela kupeleka mtendele pajio. Sindidabwele kupeleka mtendele nambo chikwanje. 35Pakuti ndidabwela kumpeleka mundu wa kangane nda atate wake, ndi mwali zidi ya mai wake, di mpongozi zidi ya apongozi wake. 36Oipa wa mundu siwakale ndiyuja wa mnyumba mwake.37Iye walionje wakonda atate kapena amai kuposa kupita ine mmene. 38Iye aliyese siwalole siwalole kunyamula msalaba ndi kunichata ine wafaa. 39Iye uyosiwa funechikalidwe siwataze nambo iye uyo siwayataize kalidwe panda ndeyanga siwayapate.40Iye uyosiwakalibishe wanikalibisha wanikalibisha ine, ndi iye uyo siwanikalibishe ine wamkalibishe uyo wanituma ine. 41Ndi iye uyosiwakalibishe mlosi pandande ndi mlosi sialandile poto ya mlosi. Ndiiye siwakalibishe walindihaki pandande ndi mundu wa uzene siwalandile mboto ya mundu wa uzene.42Walionje uyosiwamnikhe moji wa wana yawa, ata chikombe cha maji ya kumwayo zizila, pandande iye ndiopuzila, kweli ndikuzani, iye siwakoza kulepela panjila yalionje mboto yake.

Chapter 11

1Idali pambuyo pa kuwa jiwiche ochefile wake kumi ndi aili wade chokepo kupita kuyaluza ndi kukambilila mkati mwa miji yao. 2Ndi Yohana walimomapidwa pamene wadevela wa pamwamba pa vichifu ya Kristo wadepeleka utenga kupifila ochatila wake. 3Ndi ade mfundo, "iwe nde yuji wa kuja kapena walipo mwene vyembekeza kumpenyelela?"4Yesu wade yauke ndi kwa kembille mapifani onkambile Yohana yaja mu yaona ndi yaju muyavela. 5Wantu siapenya apeza kupenya osaende aeyonda amakate alama osa vecho avecha amwalile azuko kupeza umoyo nde ofuno za bwino apelekedwa nkani za bwino. 6Ndi wapeza mwausi mmeneyo walibe menta pakati paine.7Pakati pa wantu yawa adechoko Yesu wade yamba kukamba ndi guru pa mwamba pa Yohana, "Nampo ndapita kupenya pakati pa mtetete bango livulizidwa ndi mpepo?" 8Nampo chiyani nde pita kupenya muntu wadevela nchalu za zene zene achemeneo avala nchenzo wale akale pakati panyumba za mafuru.9Nampo choke kupenya chiani ndi olofa. 10Uyu ndi mmeneyo waladelembedwela penyani ndi mtume mtenge wampa pamaso pamaso yako mmesiwa chila yako pachogoro pako.11Ine ndikukambilani uzene pakatikati ache ame abadwa ndi waachikazi palibe waliwa mkuhe kupunda Yohana obatiza nampo uyo wali wamng'ono paufuru wa kumwamba ndi wa mkuru kupunda iye. 12Kuchokela siku za Yohana matizaji mpaka lelo, Ufuru wa kumwamba ndi wa mpavu ndiwa ntu ali ndimpavu amautenga kwa mpavu.13Chifuko cha olota ndi lamulo amalota mpaka kwa Yohana. 14Ndingati mlitayari kuvemela uyo ndi Eliya yuja wakuja. 15Walindi makutu yovela wevele.16Nichilinganiche ndi chiyani mbadwa izi? Ndi chifanizi chawana asewela kumsika okale ndi kupatana. 17Ndikukamba fide abule ngoma sinde vine kala kachete simdalile.18Chifukwa Yohana siwadaje popamba kudya mkate kapena kunwa mvinyo ndi pamenepo amakamba walindi vizuke. 19Mwana wa wantu Adamu wadaja ndiwamwa ndi wadya adekamba penyani ndi muntu wa kudya ndi kuhojela bwenji wa wantu alendila msomelo ndi wantu ali ndi machimo nampo ulemo uli mkati mwa vichito vake.20Yesu wadayamba kuikanize miji yimene ideha ndi vichito iva mbwino chifukwa cha salapa. 21Shauli lako, Kolazini, kaya esaide ngandu vochita va vikulu vikachitika yapa okad lepa kalekale kwa kuvala masako ndi kuchipurupusa choso. 22Nampo sikale kudeka msimo kwa jilo ndi Sidoni ntawi ya lamlo kuliko kwao.23Iwe Kapernaumu uganize si ukwezedwe mpaka kumwamba? Tyai siuchichidwe mpaka pachi pajiko ngati kwa Sodoma kudeka chitika vichito vabwino ngati umoyade chisidwir kwalwe kade kalapo mpaka lelo. 24Chabwino kwaine kuti siale chintu cha mlange jiko la Sodoma kwino ndawi ya lamulo ya kupunda iwe.25Pakati pantawi imeneyo Yesu wadakamba ndi kukweza iwe tate wa kumwamba ndojiko chifuko udawabisa mau yaya wantu ojiwa ndikuya masula kwa osusome ngati wana wanjono. 26Atefe chifuko idekukondelani imwe pamaso pano. 27Nkani senche zapelekedwa kwaine kuchovela kwa atate ndipalije wa mjiwa mwano ikupanda ataje dipulije wa mjiwa tafe popande mwana ndi waliyonche mwana wafuna kummesulila.28Majani kwaine anyifumwe mwa onche mulindi mavuto ndi mwalemeledwa ndi akafundu nanencho sindu kupulincheni. 29Jipacheni mtima wanga ndi mji yauze kuchokela mwa ine chifukwa chaine ojichiche, wakechete wa mtima ndi simpaze kupumulila kwa melo yanu. 30Chifuko mtima wanga ndi kafundu wanga osalemela.

Chapter 12

1Nyengo imeneyo Yesu wadapita siku ya sabato kupitila mminda. opuwaila wake adali ndi njala ndeanda yamba kutyola viputu ndi kudya. 2Nampho Mafarisayo yapo adapenya yayo adamkambila Yesu, le penya opunila wako awananga matauko achita siku yayo siyafunika siku ya sabato.3Nampho Yesu adamkambila, "simeasome umo Daudi yayo wadayachita nyengo yapo wadali ndi njala, pamojhi ndi wandhu adali nalo? 4Umo wadelowla mkati mwa nyumba ya Mulungu ndi kudya mikate yolangizila yayo yadali osati tauko kudya ndi onyiwajha adalinao, nampho tauko kwa anchembe?5Mkali simdasome malamulo, yakuti pasiku ya sabato anchembe mkati mwa nyumba Mulungu omawananga sabato nampho alijhe cholakwa? 6Nampho nikamba kwa anyiimwe kuti uyu wali wamkulu kupunda uyumba ya Mulungu walipano.7Ngati mdakajhiwa iyi itandauza chiyani, ndifuna lisungu ndi osati nchembe; sinidakawa lamulani opande ndi kulakwa. 8Pakuti mwana wa Adamu ndiye wa mkulu wa sabato."9Ndipo Yesu wadachoka pajha wadapita msinagogi yao. 10Penyani kudali ndi mundhuopoleza jhanja. Mafarisayo adamfujha Yesu kukamba u bwanji ndi cholungama kulamicha siku ya Sabato? Kuti akoze kumwimba mlandu kochita machimo.11Yesu adamkambila, "yani mwa anyiimwe uyo wali ndi mbelele mmojhi, uyo mbelele wakagwela mkati mwa jhenje siku ya sabato siwamgwila ndi kumchocha kwa mbhavu mkati mwa jhenje? 12Bwanji ndi chiti cha mtengo kupunda nditu, osati kupunda mwa mbelele! Kwa icho nde mbaa kuchita vabwino siku ya sabato."13Ndipo Yesu adamkambila yujha mundhu "tambasura jhanja lako" wadatambasura ndi kupeza kulama ngati ujha wena. 14Nampho Mafarisayo adachoka kubwalo kukonja ntundu wa kumpweteka adapita kubwalo kukonja ntundu wena. Adati mkufunafuna ntundu wa kumpha.15Yesu yapo wadazindikila ili wadachoke pamenepo. Wandhu ambili adamchata ndi kuwalamicha wonche. 16Adawatumiza asadajha kumchita wajhiwike kwa wena. 17Kuti kwanile ijha zene, idali kukambidwa ndi olosa Isaya, kukambe,18Penyani mtumiki wanga, namaghula okondedwa wanga. Mwaiye mtima wanga wakondechadwa. Siniuike mzimu wanga pamwamba pake. ndi kulonjeza siwalatikile malamulo kwa mayiko.19Siwavutike kapena kulila kwa mphamvu; wala waliyenche kuvela kuvela sauti yake mmiseo. 20Siwalityola bango losutulidwa; mpakana chikujho chalichonjhe icho chichocha mauchi, mpakena yapo siwapeleke malamulo ndi kukoza. 21Ndi ajhiko siakale ndi popande mantha mwa jhina lake.22Mundhu mwena osapenya ndi osakamba uyo wa kweleecha viwanda wadapelekedwa pachongolo pa Yesu. Wadamlamicha pamojhi ndi yochokela ya kuti mundhu osakamba wadakamba ndi kupenya. 23Gulu lonche lidadabwa ndi kunena "ikoza mundhu uyu kukala mwana wa Daudi?"24Nampho nyengo Mafarisayo yapo adavela chidabwicho ichi adanena, "uyu mundhu siwachocha vilombo kwa mphamvu zake mwene ikapanda kwa mphamvu za Belzebuli, kwa mkulu wa vilombo." 25Nampho Yesu wadajhiwa maganizo yawo ndi kwa kambila, "ndipo ufumu uwo wa patulana wene uwanangika, ndi kila mujhi kapena nyumba ijhipatula yene siima."26Ikakala Satana siwamchoche Satana, ndipo wajhikonja pa malo pake mwene. 27Ndi ntundu uti ufumu wake siuime? Ndi ngati nichocha vilombo kwa mphavu za Belizeli, ochata wanu siachoche kwa ili si akale olamula wanu.28Ndi ngati nichocha chilombo kwa mphavu za Mzimu w Mulungu, ufumu wa Mulungu waja kwanu. 29Ndi mundhu siwakoze bwanji kulowa mkati mwa mnyumba ya mwene mphamvu ndi kuba, popande kummanga wati ndi mphamvu poyamba? Ndipo siwabe vinhu vake kuchokela mkati mwa nyumba. 30Waliyenche osakale pamojhi ndi ine walikumbuyu kwa ie ndi iye osasoghaniche pamojhi ndi jhe mmeneyo wa mwaza.31Kwa icho ninena kwanu, kuti chimo ndi kupepula wandhu siwalekeledwe, ikapanda kumpepula Mzimu Oyera siwalekeleledwa. 32Ndi waliyonche wanena mau kumaungulila mwana wa Adamu, limenelo siwalekeledwe. Nampho waliyenche siwanene kozungulila ndi mzimu oyela, mmeneyo siwalekeleledwe, pajhiko lino, ndi ilo likujha.33Kapena uchite mtengo kuti ukale wabwino ndi chipecho chake cha bwino, kapena uwanange mtengo ndi chipacho chake, pakuti mtengo ujhiwike kwa chipacho chake. 34Anyiimwe chibadwa cha njoka, anyiarwe ndi owanangika. Mkoza bwanjikunena vichito vabwino? Pakuti pakamwa panena kuchokela musangila yayo yalimo mutima. 35Mundhu wabwino masungila nawake mwa bwino mwa mtima wake kuchoka ya bwino, ndi mundhu oyipa masungila choipa cha mtima wake, chichocha chili choipa.36Ndikukambilani kuti mmasiku ya kulamula wandhu siachoche zowalega za mau ilo lopande mate mwalikamba. 37Pakuti kwa mau yako siuwelengedwe malinga ndi kwa mau yako siulangidwe.38Ndipo akumjhi wa olemba ndi Mafarisayo adamuyankha Yesu ndi kunena, "opunzisi tidakakonda kupenya zizindikilo cha Yona olosa." 39Nampho Yesu wadayankha ndi kwakambila, chibadwa choipa ndi cha chigololo chifuna vizindikilo. Nampho popande chizindikilo sichichochedwe kwa anyiiwo popande chijha chizindikilo cha Yona olosa. 40Ngati mujhe olosa Yona umoloadali mkati mwa mwinuka mwa nchomba ya iklu pa masiku ya tatu usana ndi usiku.41Wandhu wakuninawi si aime pachogolo pa kulangdwa pamojhi ndi chibadwa cha wandhu yawa ndikuchi langa. Pakuti adelapa kwa ulaliki wa Yona, penyani mundhu mwena wa mkul kusiyana ndi Yona walipano.42Mkati wa Mfumu wa kumwela siwaime pa chilanga pamojhi ndi wandhu achibadwa chino ndi kuchilanga. Wadajha kuchokela kuchokela motela mwa jhiko kubwela kuvecheta ulemu wa Selemani ndi kapenyani mundhu mwena wamkulu kupunda Seleman walipano.43Nyengo chilombo choipa chimchoka mundhu, chipita pamalo popande ndi majhi ndi wafuna kupumulila, nampho siwapaona. 44Ndipo wanena sinibwele myumba yanga iyo nachoka. Wakabwela kupeza ijha nyumba yalambulidwa ndi yatokala moyembekeza. 45Ndipo wapita kuwatenga wena mizimu yoyipa saba, yano aliwoipa kupunda iye. Kubwela kukala wonche pajha. Ndipo kalo lake lotela kukala loyipa. Kupambana lo yamba nde umusikalile kwa chibadwa chino choipa.46Nyengo Yesu yao wadali kukambana ndi gulu penyani amanyi wake ndi achabale wako adaima kubwalo, afuna kukamba naye. 47Mundhu mmojhi adamkambila, "kapenya amayi wako ndi achabale wako ayima kubwalo, afuna kukamba ndiiwe."48Nampho Yeu wadayankha ndi kwa kambila, uyo wadamjhiwicha, "amanyi wanga ndi yani? Ndi achabale wanga ndi achiyani?" 49Iye, wadatambasura jhanja lake kwa opuuzila wake kunena, "penyani anyiyawa nde amaye ndi achabae wanga! 50Pakuti waliyenche wachita achikondi va atate wanga alikumwamba, mundhu mmeneyo ndiye mbale wanga, mlongo wanga ndi amaye wanga."

Chapter 13

1Pa siku lija Yesuwadachoka pakomo ndi kukala m'bali mwa nyanja. 2Gulu la likulu la wanthu lidamzungulla, wadalowa m'bwato ndi kukala mkati mwake gulu lonche lidaima m'bali mwa nyanja.3Ndipo Yesu wadakamba mau yambili mwa chilangizi, wadakamba penya , ovyala wadapita kuvyala. 4Yapo wanavyala mbeu zinjake zidagwela m'bali ya njila mbalame zidaja kuzizopola. 5Mbeu zina zidagwa pamwamba pa mwala, zisizidapez doti lokwana mwa chizulumukila zidapuka ndande doti lidali lochepa. 6Nampho jua yapo lidawala lidapyelela ndande zidalibe mizo zidauma.7Zina zidagwa pakati pa mitengo ya minga, idatalika ndi kuipitilila . 8Zina zidagwa pa doti la bwino ndi kubala mbeu, zina makumi sita ziba makumi yatatu. 9Uyo walindi makutu wavele.10Opunzila wake adaja ndi kumkambila Yesu ndande chiyani ukamba ndi watu kwa chilangizi. 11Yesu wadayankha ndi kuakambila mwakondendwa ndi kupachidwa kujiwa chisisi cha ufumu wa kumwamba nampho kwa inyiio sadapachidwe. 12Nampho walionche walinacho iye siwaonjezewe kupunda ndi siwapate pindu lalikulu, nampho uyo walibe kanthu hata chija walinacho siwalandidwe.13Kwa icho nikamba nao mwa chilangizi ndande ingakale apenya sadapenya uzene, ndi ingakale avela sadavela ndi kujiwa. 14Ulosi wa Isaya wakwanila kwa anyiio, uja ukamba, "yapo mvela mvela nampho vili vonche simwanavo, nyengo mpenya, penyani nampho kwa ntundu ulionche msadajiwa.15Ndi mjutima ya munthu yawa yakala mdima ndi olimba kuvela ndi atimila maso yao, kuti asadakoza kupenya kwa maso yao. Kapena kuvela kwa makutu yao ndi kujiwa kwa mitima yao, kwa icho adakani ng'anamuklancho mdaka achilisa.16Nampho maso yanu yadalisidwa ndande yapenya ndi makutu pakuti yavela. 17Zene nikukambilani alosi ambili ndi wanthu amalinga adali ndi ndi kumbilo la kuviona vinthu mviona anyiimwe ndi saadakoze kuviona, adakumbila kuvela vimene mvela anyiimwe nampho saadavele.18Chipano velani chilangizi cha ovyala. 19Walionche wavela yapo wavela maula ufumu ndi siwadalijiwa, ndipo satana wakuja ndi kunyakula chija chatovyalidwa mkati mwa mtima wake. Iyi nde mbeu ijayavyalidwa m'bali ya njila.20Mbeu yavyalidwa pa mwala ndi munthu yuja wavela mau ndi kulilandila kokondwelela mwa msanga. 21Wakali walije mizo mkati mwake walimbikila pa nthawi yaifupi, mavuto yakachokela kukuza mau wajikuwala kwa chizulumukila.22Wavyalidwa pakati pa mitengo ya minga nde yuja wavela mau nampho masauk ya mjiko ndi chinyengo cha chuma chilizungulila mau lisadabala vipacho. 23Wavyaldwa pa doti la bwino, nde yuja wavela mau ndi kulijiwa, huyu nde yuja wabala vipacho ndi kuendekela kubala imoji kupunda makumi kumi, na makum sita ina makumi matatu.24Yesu wadaapacha chilangizi china ndi kuakambila ufumu wa kumwamba ufanana ndi munthu wada vyala mbeu ya bwino mmunda wake. 25Nampho wanthu yapo adaojela, mdani wake wadaja kuuyala changala pakati pa ngano ndi mwene kuchokapo. 26Pambuyo ngano yapo idabuka ndi kubala, ndipo machangale nayo yadapuka.27Atumiki a mwene munda adaja ndi kumkambia "achimwene" simdavyale mbeu ya bwino mmunda wanu? Ikala bwanji uli ndi machangale? 28Wadaakambila mdani nde wachita ichi. atumiki adamkambila, ""kwa icho ufuna tipite tiayazule?29Mwene munda wadakambila iyayi yapo simzule machangale sizula ndi ngano. 30Yasieni yakule pamoji mbaka nyengo yo goola, nyengo yogoola sindikambe kwa ogooa, poyamba zulani machangale muyanange mitolo mitolo ndi kuyabucha, nampho kokolelani ngano mnkhokwe yanga.31Ndipo Yesu wadaachochela chilangizi chinandi kuakambila "Ufumu wa kumwamba ufanana ndi mbeu ya haradali iyo munthu watenga ndi kuvyala mmunda mwake. 32Mbeu iyi nde yaing'ono kulekana mbeu zina zonche. Nampho ikamela ikala mtengo mbaka mbalame zikuja kumanga visa munthawi zake"33Wadaakambila chilangizi chinancho "Ufumu wakumwamba ndi ngati ya idatengedwa ndi wamkazi ndi kuisingizana ndi vitatu va ufa mbaka vitupane.34Vonchevo Yesu wadavikamba pagulu pagulu kwa vilangizi ndi popanda vilangii siwadakambe nao chilichonche. 35Iyi idali kuti chija chidatokambidwa kupitila kwa mlosi chikoze kukwanila, paja wadakamba, sindi panule kukamwa kwanga mu chilangizi, sindikambe vinthu vya vidabisidwa chiyambile mapingidwe ajiko."36Yesu wadausiya msonchano ndi kupita kukomo opunzila wake adampitila ndi kukamba, "titandauzile chilangizi cha machangale mmunda." 37Yesu wada ayankha ndi kukamba wavyala mbeu ya bwino ndi Mwana wa Adamu. 38Mundi ndi jiko la pauchi, ndi mbeu ya bwino nde wana a ufumu, machangale ndi wana a mdani ndi mdani iye wa vyala ndi satana. 39Kukolola ndi kutela kwa jiko ndi okolola ndi anjelo.40Ngati muja machangale yakokoledwa ndi kubuchidwa moto ndimo siikalile kuleta kwa jiko. 41Mwana wa Adamu siwaatume angelo wake ndikukusa kuchoka mu ufumu wake vindu vonche vachiticha machimo ndiao achita volakwa. 42Saataye oriche muuvumi wa moto, kumene sikukale malilo ndi kugaya mano. 43Ndipo wanthu amalinga saakale oyela ngati jua mu ufumu wa atate wao iye wali ndi makutu ndi wavele.44Ufumu wa kumwamba ndi ngati yoikilidwa iyo yabisidwa mmunda. Munthu wadaiona ndi kuibisa. Mwachi kondelelo chake wadapita kugulicha vonche ivo wadalinavo ndi kugula munda. 45Ufumu wa kumwamba ncho ndi ngati opanga malonda uyo wafunafuna ya mtengo wa pamwamba. 46Yapo wadaiona ija yamtengo wa pamwamba wadapita kugulicha kila chinthu wadalinacho ndi kuigula.47Ufumu wa kumwamba ndi ngati koka lili mkati mwa nyanja, nde kutili kusa vipangidwe va kila mtundu. 48Yapo lidajala ovua adaliguzila kutunda nde adakala panchi ndi kukusa vinthu va mate ndi kuviia mvinthu , nampho vopande mate adavitaja kwa kutali.49Siikale chimwechi motela kwa jiko, angelo saaje kuachocha wanthu ochimwa mwa wanthu amalinga. 50Ndi kuataya mkati uvumi wa moto nd sikukale chililizi ndi kugaya mano.51Mwajiwa vinthu vonchevi? Opunzila adamyankha "yetu." 52Yesu wadaakambila mlembi waliyonche wali opunzila wa ufumu wafanana ndi mwene nyumba wachocha muyake vinthu vichipanondi vakale. 53Idali Yesu yapo wadata vilangizi vonchevo wadachoka bendeka limenelo.54Ndipon Yesu wadafika mu chigao chake ndi kuayaluza wanthu mu masinagogi , zochalila ndi kuti adadabwa ndi kukamba . 55Munthu uyu opande mwana wa Mariamu asati amai wake? Ndi abale wake osati, Yakobo,Yusuph, Simoni ndi Yuda? 56Ndi achialongo wake sitilinao pampano patu? Nkha munthuuyu wapata kuti vonchevi?57Wadaapicha, nampho Yesu wadaakambila mlosi siwapepulidwa nampho kukoo kwao ndi kujiko lao. 58Ndi siwapange vambili ndande adalibe chikulupi ndi iye.

Chapter 14

1Kwa nyengo imeneyo, Herode wadavela nkhani pakati pa Yesu. 2Wadaakambila atumiki wake "uyu ni Yohane mbatizi wahyuka kuchoka kwa akufa kwa chimwcho mphavu izi zilip[o pakati pake."3Pakuti Herode wadamgwila Yohane ndi kummanga ndi kumtaya m'boma kwa ndande ya Helodia, mkazake wa Filipo mkulu wake. 4Pakuti Yohane wadamkambila, "opande bwino kumtenga iye kukala mkazake." 5Herode wadakampa nampho wadaaopa wanthu kwa chifuko wadamuona Yohane kuti olosa.6Nampho, nyengo siku lobadwa Herode yapo idafika mwana wa Herode wadavina pakati kti pa wanthu kumkwadilicha Herode. 7Pakati pa kuyankha kili kw chilanga kuti siwampache chalichonche icho iwapemphe.8Pamalo poyamikidwa ndi amake, wadakamba, "nipache ine pano katika kombe mutu wa Yohane m'batizi." 9Mfumu wadali ndi dandaulo kwa mapemphelo ya mwali, nampho kwa chifuko cha chilango chake, kwa ndande ya onche anyiyao adali pachakudya pamojhi ndi iye wadalamula kuti ifunika ichitike.10Wadatumiza Yohane watanidwe kchokela m'boma. 11Kuti wadulidwe mutu wake ndi udapelekedwa pakati pa sinia ndi wadampacha mwali wake ndi wadaupeleka kwa amake. 12Pambuyo pake opuzila wake adajha kulitenga nthupi ndi kulizika, pambuyo pa ili adapita kumkamila Yesu.13Ndipo Yesu yapowadavela yaya, wadaipatula kuchoka pamalo pajha wadakwela mkati mwa thanga wadapita kumalo yayoyadakonjedwa, nyengo msonkhano yapoudajhiwa ukowadali, adamchata kwa myendo kuchokela mmijhi. 14Ndipo Yesu wanajha pachogoopao wadauona msonkhano waukulu wadauonela lisungu ndi kuwalamicha matenda yao.15Ujulo yapoudakwanila, opuzila adajha kwa iye ndi kukamba, "yaya ni malo ya ndi masiku tayali yakwanila. Kuwatumiza msonkhano kuti apite mmijhi akagule chakudya kwa ndande ya anyaiwo."16Nampho Yesu wadaakambla, "alibe ndande yopita kwao, apacheni namwe chakudya," kwa ndande yao. 17Wadaakambila, "pano tilinayo mikate isano ndi nchomba ziwilipe." 18Yesu wadakamba, "jhanayoni kwanga."19Potela pake Yesu wadaulamula msonkhano ukale panchi pamaujhu. Wadaitenga mikate isano ndi nchomba ziwili wadapenya kumwamba, wadapemphela ndi kudula mikate wadaapacha opuzila. Opuzila adaupacha msonkhano. 20Adadya onchendi kukhuta pambuyo adavisonkhanicha vipande vonche va chakudya ndi kujhaza miseche kumi ndi iwili. 21Anyiwajha anyiyao adadya wadapimila kuti wa achimuna elfu zisano popande kuwawenga wa achiazi ndi wana.22Mala kamji wadaalamula opozila alowe mkati mwa thanga, nyengo imeneyo iye wadaulaila msonkhano upite kumijhi yao. 23Pambuyo pa kuuaila msonkhano ndi kuchoka, wadakwela pamwamba pa pili kupempha yoka. Nyengo yapokudali ujhulo wadali kumeneko yokha. 24Nampho saino thangayapo lidali pakatikati pa nyanja lidapepesuka pepesuka kwa ndande ya mafunde, pakuti mphepo zidali zo siyana siyana.25Pakati pa usiku wa Kanai Yesu wada enda pamwamba pa majhi. 26Nyengo opuzila wake yapo adamuona niwaenda pamwamba pa majhi, adaopa ndi kukambani "chihyuka" ndi kukweza mau yao pakati pa mantha. 27Yesu wadaakambila mala kamojhi, wadakamba "jipacheni mtima," ndi ine! Msadaopa.28Petro wadamuyankha ndi kukamba, "ambuye ngati ndi imwe, nilamuleni nijhe kwanu pamwamba pa majhi." 29Yesu wadakamba, "majha" chimwecho Petro wadachoka mkati mwa thanga ndi kwenda pamwamba pa majhi kumchata Yesu. 30Nampho Petro yapo wadayaona mafunde, wadaopa, ndi kuyamba kubila panchi, wadatana kwa mphavu ndi kukamba, "ambuye nilamicheni."31Mwa msanga Yesu wadanyosha jhanja lake wadamnyakula Petro, ndi kumkambila iwe mwene chikulupi chochepa, ndande yanji udali ndi mantha? 32Yesu ndi Petro yapo adalowa mthanga, mphepo idalapa kupuputa. 33Opuzila mthanga adamgwadila Yesu ndi kukamba cha zene iwe ni mwana wa Mulungu.34Ndi yapo adatoyomboka, adafika kujiko la Genesareti. 35Ndi wanthu pakati pamalo yajha yapoadamjiwa Yesu, adatuma uthenga kila pamalo pa chidya, ndi kumpeleka kila uyo wadali odwala. 36Adamsihi kuti ukoza kuliguula lake, ndi ambili yao adaligwila adalama.

Chapter 15

1Ndiyapo Mafarisayo ndi olemba adaja kwa Yesu kuchoka Kuyerusalemu, ndikamba. 2Ndande yanji opuzila ayawananga mlandilidwe ya azee? Pakuti sasamba mmanja mwao yaoakuja chakudya. 3Yesu wadayankha ndikwakambila, "anyiimwe, ndande yanji mniwangila lamulo la ambuye kwa chifuko chamalandilidwe yanu?"4Pakuti Mulungu wadakamba, mlemekeze ambuye wako ndi amai wako, ndi uyowakamba mtila kwa ambuye ndi amai wake hakika siwafa. 5Nampho anyiimwe mukamba kila wamkambila atate wake ndi amai wake, "kila mtandizo ambao siwafute kuchoka kwanga chipano ndi mphaso kuchoa kwanga." 6Muntu mmeneyo walibehaya kumlemekeza ambuye wake. Katikanamna ii mjiwa mau la Mulungu kwachifuko ya malandilidwe yao.7Anyiimwe anafiki ndi bwino Isaya umowadalotela pamamba panu yapowadakamba. 8Wantu yawa sianilemekeza ine kwa mmakamwa mwao. Nampho mitima yao ili patali ndiine. 9Aniabudu bure, kwa chifuko ayaluza mayaluza yayoadaagiza ndi wantu.10Ndiyapo adatana makutano ndi kwakambila, "velani ndi mjiwe. 11Palibe chintu chilowa mkamwa mwa muntu ndi kumchita najisi ila chija chichoka mkamwa ichi nde chi mchita muntu kukala najisi."12Ndiyapo opuzila adamuendela ndikukamba ndi Yesu, bwa ujiwa Mafarisayo yapoadavela lija mau adaipidwa. 13Yesu wadayanka ndikukama, "kila mmea ambao ambuye wanga akukamba siadavyale siuzulidwa. 14Asieni oka, anyiio ndi viongozi vipofu, ngati kipofu siwamchongoze kipofu mnjake onche awili siagwemjnje."15Petro wadyanka ndi kwakambila Yesu, "tikambile mfano uu kwatu." 16Yesu wadayanka, "namwe mkali simuelewa.?" 17Anyiimwe simuona kuti kila chipita kmwa chipitila mmimba ndi kupita kuchimbuji?18Nampho vintu vonche vichoka mkamwa vichoka mkati mwa mtima nde ivo vintu vimtila muntu unajisi. 19Pakuti katika mitima ichoka maganizo yoipa, kupachigololo, uasherati, unkungu, kushuhuda mtila ndi matukwano. 20Yaya nde vichito vimtila muntu unajisi, nampho kudya bila kusamba mmanja sikumchita muntu kukala najisi.21Ndiyapo Yesu wadachoka pamalo paja ndi siwajisanke kuelekea pandeza majiko ndi Sidoni. 22Penya wadaja wamkazi Mkanani kuchoka pande zimene. Wadakweza sauti wadakamba, "nilengere, ambuye mwana wa Daudi binti wanga watesedwa sanandi mashetani." 23Nampho Yesu siwada yanke mau opuzila wake adaja ndi kumtondoza, adakamba, "mchocheni wapite zake, chifuko watitimbila kelele."24Yesu wadayanka ndikukamba, sinidatumidwe kwa muntu waliyonche, ingakale kwa mbelele ayiyao ataika kunyumba ya Israeli. 25Nampho wadaja ndikukwatama pachongolo pake, wadakamba, ambuye nitandizeni. 26Wadamuyanka ndikukamba, "osati bwino kutenga chakudya chawana ndi kwataila agalu."27Wadakamba, "etu ambuye, atachimwecho agalu waang'ono kudya chakudya chikugwa pameza pa ambuye wao." 28Ndiyapo Yesu wadayanka ndi kukamba, "wamkazi, imani yako ndi eikulu ndiichitike kwako ngati umoufunila, "ndi biti wake wadali walamichidwa katika nyengo imene.29Yesu wadachoka pamalo paja ndikupita pafupi ndi nyanja ya Galilaya potela wadapita pamwamba pa pil ndikukala kumwe. 30Kundi lalikulu lidaja kwake ndikumpelekela viwete, vipofu, mabubu, vilema ndi winawina, adali odwala adaika mmyendo mwa Yesu ndi kuwalamicha. 31Nalo gulu adazizwa yapoadapenya mabubu naakamba ndi vilema adachitidwa alama, ndi viwete amaenda ndi vipofu amapenya, adamuyamika Mulungu wa Israeli.32Yesu wadatana opuzila wake wadakambila, "nawaonela lisungu umati, kwachifuko ali ndiine kwa siku zitatu bila kudya chintu chalichonche sinalaila apite kwao bila kudya, sadaja kuzimia munjila." 33Wopuzila wake adamkambila, "nikuti tikozakupata mikate yaktikwana yapa nyikani kukuticha gulu lalikulu chimwechi?" 34Yesu wadakambila, "muti ndi miate iingati?" Wadakamba, "saba ndi nchomba zazing'ono zochepa." 35Yesu wadalamula gulu likale panchi.36Adatqa ija mikate saba ndi nchomba, ndi baada yakuyamika, adaidula ndi kapacha opuzila opuzila adapacha gulu. 37Wantu onche adadya ndi kutosheka, ndi adakusanye makombo ya vipande va vakudya ivovidakala vipande vipande, vidajala miseche saba. 38Onche anyioadadya adali wachimuna elfu zinai bila wachikazi ndi wana. 39Potela Yesu wadalilaila gulu apite zao ndi wadalowa mkati mwa masha ndi kupita sehemu za magadani.

Chapter 16

1Mafarisayo ni Masadukayo, adamjela ndi kumuyesa Mpulumusi walangize langize lachoka kumwamba. 2Nampho Mpulumusi wadayankha ni kwakambila kuti, "ikakala iyulo mkamba kuto hali ya hewa ni yabwino pakuti kumwamba ndikofuwila."3Niumawa mkamba, "hali ya hewa lelo osati ya bwino pakuti kumwambandikofuwila ni mitambo ya vini kila jiko lonche." Mjiwa kutadauza ubwino wa jiko, nampho simkoze kutandauza alamaza nthawi. 4Chibadwa choipa nicho chigoolo chifuna langizo, nampho paliji langizo lalilonche chipachidwe, ikapanda lija la Yona. Badae Mpulumusi wadaleka ndi wadapita zake.5Opuzila adaja upande wa kawili, nampho adali ayawalila kutenga mikate. 6Mpulumusi wadakambila "jipenyeleleni ni mkale ojiwa ni voipa va Mafarisayo ni Masadukayo." 7Opuzila adafunchana achinawene ni kukamba, "ndi kwa ndande tidatenge mikate." 8Mpulumusi wdajiwa limenelo ni wadakamba, "anyiimwe muli ni chikulupi cha ching'ono, ndande chiani mwaganize kukambichane mwachina wene ndi kukamba kuti ndikwande mdatenge mikate?"9Bwanji mkali simjiwa wal simkumbuka ija mikate isano kwa wanthu elfu zisano, ndi miseche ingati mda kusanya? 10Au mikate saba kwa wanthu elfu zinai, ni niseche ingati mdatenga?11Ikala bwanji kuti ata simwelewa kuti midali sinikamba namwe juu ya mikate? "Mjiponyelele ni mkate maso ndi voipa va Mafarisayo ni Masadukayo." 12Pambuyo adajiwa kutiwadali siwakambila juu ya kukala maso ndi mikate ili yo wawa, ila kukala maso ni mayaluzo ya Mafarisayo ni Masadukayo.13Muda Mpulumusi wafika sehemu ya Kaisaria ya Filipi, wadafuncho opuzila wake, wadakamba, "wanthu akamba kuti mwana wa munthu ndiyani?" 14Adakamba, "wina akamba kuti ni Yohane mbatizaji wia, Eliya: ndi wina, Yeremia, mmojiwpo wa mlose. 15Wadakambila, anyiimwe mkamba ine ndiyani?" 16Kuti wakayankha, Simoni Petro wadakamba, "iwe ni Mpulumusi mwana wa Mlungu wali wamoyo."17Mpulusi wadamyankha ndikumkambila, "wadalisidwa iwe, Simoni Bar Yonapakuti mwazini nyame vida kuvunukulile ili, ila atatawanga ali kumwamba. 18Nane pa nikukambila kuti iwe ndi Petro, pani pamaemba pa pili ili ilimange kanisa langa, ndivicheko va mzimu oipas sivilioza.19Nikupache iwe funguo za ufumu wa kumwamba. Chalichonche uchimangile panchi chikale chamangidwa kumwamba, ndi chalichonche uchimaule panchi chimasulidwe ndi kumwamba." 20Baadae Mpulumusi wadalamula opuzila asamkambila munthu waliyonche kuti iye wadali ni Mpulumusi.21Tangu wakati umeneo Mpulumusi wadayamba kwakambila opuzila kuti ndi lazima wapite Kuyerusalemu, kuzunjidwe kwa mambo yambili katika manja ya azee ni wakulu anehembe ni otenga nkhani, kupedwa ndi kuhyuka siku ya katatu. 22Pambuyo Petro wadamtanga Mpulumusi pampepete ni kumkalipila, kokamba, "jambo ili ndi likale patali ndi iwe ambuye, ili lisachokela kwa iwe. 23Nampho Mpulumusi wadang'anamuka ni kumkambila Petro, "bwela kumbuyo kwanga satana! Iwe ndi chizuizi kwa ine, kwa ntando siujali mambo ya Mlungu, ila mambo ya wanthu"24Baadae Mpulumusi wadakambila opuzia wake, "ngati munthu waliyonche wakafuna kumchata ine, ndi lazima wajikane iye mwene, wautenge mtanda wake, ndi wanichate." 25Pakuti uyowafuna kuyalamicha maisha yake wayapoteze,ndikwa waliyonche wayopoteza maisha yake kwa chifuko changa wayalamicha. 26Bwanji ndi pindu lanji walipate munthu wakapa jiko lonche nampho wakapoteza umoyo wako? Bwanji ndi chinthu chanji wachoche munthu katika kubadilishana ndi moyo wake?27Pauti mwana wa Mlungu wabwela katika ufulu wa atata wake ndi angelo wake. Nae siwamlipe kila munthu kulinganandi vichito vake. 28Zene nikukambilani kuli wina wanu mwaima ambao simulawa nyifa mpaka mkamuona mwana wa Mlungu ni waja katika ufumu wake.

Chapter 17

1Siku sita pambuyo pake Yesu wadatenga pamaji ndi Petro, ndi Yakobo, ndi Yohana m'bale wake, ndi wadateng mpaka pamwamba pa pili lalitari anyiiwo achinawene. 2Wadabadilishidwa pachogolo pao pamaso pake padpulikila ngati jua,ndi nchalu zake zidaonekana za pulikila ngati dangalila.3Penya paja adachakila Musa ndi Eliya na akamba naye. 4Petro wadajibu ndi kumkambila Yesu, "ambuye ndi bwino kwanthu ife kunkala pamala yopa, ngati siunkumbile, sinimange yopa vibanda vitatu, chimoji chako, ndi chimoji kwa ajili ya Musa, ndi chimoji kwa ajili ya Eliya."5Nyengo ni wakamba, penya mtambo oyele udantila chi tunchi ndi penya, idacha kila sauti kuchoka mmitamba, niikamba, "uyu ndi mwana wanga akandedwa ndikandweledwa naye, mvecheleni iye. 6Opuzila yapo adavela yameneyo, adagwa liali ndi adaapa sana." 7Nde yapo Yesu wadaja wadaguso ndi kukamba, "inukani wala simdaopa." 8Naoncha adainuka maso yao kumwamba nampho siadamwane munthu ila Yesu yonkape.9Niyapo amachikakupili, Yesu wadaagiza, wadakamba, "msidachancha nkani ya kuona vimenevo mpaka mwana wa mwanadamu yapo siwauchidwe kuchoka pakati pa akufa." 10Opuzila wake adamfuncha, adakamba, "ndande chiani olemba ukamba kuti Eliya siwajehuti?"11Yesu wadajibu wadakamba, Eliya siwaje uzene ni siwabweze vinthu vonche. 12Nampho nikukambilani anyiimwe, Eliya wanthu kuja, nampho sadajiwe.Badala yake adamchitila vichito ivo amafuna anyiio. Nimchimwechoncho mwana wa mwanadamu ndiumo siwatesewe mmanja mwao. 13Ndipo opuzila adajiwa kuti wamaongea nkani ya Yohana abatiza.14Yapo adafika pakati pa gulu la wanthu, munthu mmoji wadamnchota, wadabula magoti pchogolo pake, ni kumkamila, 15"ambuye, mumuonele Lisungu mwana wanga, pakuti wali ni kifafa ni wateseka sana. Pakuti nyengo zambili wagwela pamata ama mmaji. 16Nidampeleka kwa opuzila wake, nampho sadankoze kumlamicha."17Yesu wadamjibu wadakamba, "anyiimwe chibazi sichikulupalila ni echo chawanangika, sininkale pamoji na anyiimwe mpaka sikulanji? Sinivumiliane namwe mpaka siku lanji? Mpele pano kwanga." 18Yesu wadamkalipila, ni mzimu udachoka. Mnyamata wadalamichidwa mda uuja.19Ndipo opuzila adamjela Yesu ko jibisa kumfuncha, "ndande chiyani sitidankale kumchancha?" 20Yesu wadakambila, "ndande ya chinkulupi chanu chaching'ono, uzene nikukambilani, ngati simnkale ni chinkulupi hata chaching'ono ngati punje ya mbeu ya haradali, simnkoze kulikambila pili ili, lihame kuchoka yapa lipite uka, nalo silihame ni sikunkala ni chinthu chalichonchecha cha kutokunkozekana kwanu." 21(Penya: mau ya mzele wali, "nampho, aina ii ya mzimu sinkazekana kuchoka, ila kopempha na kumanga," siyaonekana pakati pa nakala za bwino za kale).22Nyengo akali bado ku Galilaya, Yesu wadakambila wanafunzi wake, "Mwana wa Mwanadamu siwantilidwe mmaja mwa wanthu. 23Ni siamuipe, ni siku ya katatu si wa uke," opuzila adadandaula sana.24Naoncho yapo adafika Kapernaumu, wanthu akusanya kodi ya nusu shekeli adamnchata Pero ni kukmba, Bwapuzisi wanu wipa kodi ya nusu shekeli? 25Nayoncho yapo wadalowa mnyumba, Yesu wada chogolela kumfuncha ndiwakamba, uona bwanji, Simoni? Achogoleni ajiko atenga msonko kapena malipilo kwa wantu wati? Kwa achiwana wao kapena kwa alendo?26Ni nyengo Petro yapo wadakamba, "kuchoka kwa alenda" Yesu wadakambila, mchimwecho almulidwa achochedwa pakati pa lipila. 27Nampho sitidaja kuwahita achochechasagha achite vechima, pita kunyancha, penya mbeja, ndi uteng ija nchomba ije huti, baada ya kunchakula pakamu pake, siupeze muja shekeli imoji, itenge ndi uwaaninke achachecha sogho kwa ajili yanga ndi iwe.

Chapter 18

1Ntawi yomwezo oyaluzidwa adabwela kwa Yesu ndikumkambila, "yani waliwamkulu paufuru wa kumwamba?" 2Yesu wadamtana mwana wang'ono wademwika pakati pao. 3"Ndikukamba chazene ndikukambilani ngti osalapa ndikukala ngati wana wa ang'ono ang'ono simkoze kurowa kuufuru wa Mulungu."4Kwa mmwemo uyo wajichicha ngati mwana wa mng'ono muntu ngati mmeneyo ndiwa mkuru pakati kati paufuru wa kumwamba. 5Ndiwali yenche wamlandila mwana wamng'ono pa jina langa wandilandila ine. 6Nampo waliyenche siwachitiche mmoji pakati pawa mng'ono uyo avemeleza kuzukira, siikale bwino kwa mufu mmeneyo mwala wao ukuru wo pelela limangidwe mkosi mwake ndi kumbizidwa pakatikati panyanja.7Daleleo jiko chifuko chantawi yoichipidwa pakuti ilibe mate kwa ntawi zimenezo kuja nampo dale lake muntu yuja ntawi zimene sizije chifuko cheiye. 8Ngati janja lako kapena mwendo wako siuku chiti chile voipichidwa udule ndi uutaye patari ndiiwe ili bwino kupunda kwa iwe kulowa paufuru ulije janja kapena olemela kupunda kutaidwa mmoto osata uli ndi wanja ndimiendo yoche.9Ngati diso lako litakuchitiche kuipa lizule ndiulitaye patali ndiiwe ili bwino kwambili ulowe pantendele ndi diso limoji kupunda kutaidwa mmoto wasata uli ndi masoyonche.10Jipenyeni uti osakala mda mdelele jumoji wa wang'ono ang'ono yawa ili ndimate kukukambilani kumwamba kuli angolo wao siku zonche ndi aipenya nkope yaota fawanga ali kumamba. 11(Jengelelo mau ya penyekano ngati mzele 11, "pakuti Mwana wa Muntu wadefika kupurumucha chija chida taiko")12Mgani zila chiyani? Ngati muntu wali ndi mbelele mia moja ndi imoji wapoikataika bwanji si wangalisie fisiini ndi tisa mphiri ndikupita kuifuna funa imoji yataika? 13Ndiwa kaipeza, chazene ndikukambilani si wasangalale kupunda zija jisiini na fisu si zidakaike. 14Chimojimoji osati chikundi chaatate akumwamba kuti mmoji wa wang'ono yowa wa taike.15Ngati mbale wako wakakula kwila maputa ukamlangize cha lakwicho pakati pako ndiiye waliyeko ngati waka kuvecha siukale wa mbwezo mbale wako. 16Nampo ngati siwa kuvecha mtenge mbale mmoji kapena awili pamoji ndiiwe pakuti pa vamkamwa mna mboni awili kapena atatu mau lililoche likoza kugwilizika.17Ningati siwa vecha likembileni kanisa nkani imenei ningati mtundu umweo siwalivecha kanisa namwecho ngati mvutu wajiko ndi osonkecha msonko.18Zene ndikukambilani chilichonche simchimange pajiko ndiku ikwamba sichimangidwe ndilichonche simchimasule pajiko ndi kumwamba sichi maulidwe. 19Sonincho nikukambilani kuti ngati wantu awili pakati panuakavemelezana pankani iliyonche alipempa pajiko limenelo atatawanga akumwamba alichita. 20Pakuti awili kapena atatu yapo akalila limoji kwajino laine nanencho ndili pakati pao21Sonincho Petro wadabwela ndikumkambila Yesu, aakuru kangati kongati mbale wanga wakanila kwila nanencho ni mlekelele? Atakupunda mara saba? 22Yesu wadamkambila, "sindikukambila mara saba nampo ata sabini mara saba."23Kwandande imeneyo ufuru wa kumwamba ulingana ni mfuru wakuti wa mafuna kukongechela masamo kuchokela kwa akaporo wake. 24Yapo wadeyamba kukongechela masamu kaporo mmoji wadpelekedwa kwaiye mmene wadali ni ngawa ndiiye ndalama elfu kumi. 25Pakuti wadalije njila yobweza wa mkuru wake wadopeleka utenga wa gulichidwe mkazake pamoji ndiwana wake udichilichonche wadali na cho ndi maliplo ya chifike.26Mmwemo kaporo wadagwa wadachicha nibompono pachogoro pake ndi wakamba wamkume ukale ndi kuyembekeza pamoji ndiine ndi sindikulipe chilichonche. 27Mmwemo wamkuru wayuja kaporo pakuti wadakangizidwa kupunda ndi lisungu wade msilila ndi kumlekelela ngongole yake.28Nampo kaporo yuja wadechoka ndi kumpeze mojo wa akaporo anjake mmene wade mpacho ngongole, mmene wade mkongoza dineli mia wade mguza niko kumfilingoja pakosi ndi kumkambila ndi pache ngongo le ndida kukongoza. 29Nampo yaja kaporo mwijake wadagwa ndi kumpepeza kupunda ndi kumkambila ukale ndi chi yembekezo nanencho sindi kubwezele.30Nampo kaporo yuja oyamba wadekana pambuyo pake wadepita kumtaya kandende mpaka wa mbwezele ngongole yake. 31Ndeyapo adepenya akaporo aujake chimene chida chokela adadendaule kpunda nadebwela ndikumkambila waukuru wao chimene chintu chachokela .32Nde pamenepo yuja wamkuro wa akaporo yuja wademtana ndi kumkambila, "iw kaporo oyipa" ndida kulekelelaiwe ngongole yanga yonche chifuko ledawi pembelela kumpunda. 33Bwanji? Fiuda funika kukara udilisungu kwa muntu mujako ngati ine mmeme ndide kukwonda lisungu iwe?34Wamkuru wake wade kwiya ndikwa apache anyiwaja opweteka mpaka pamene siuwabweze chimene wade pachidwa chonche wadali nacho ngongole. 35Mmenemo nde atata wanga akumwamba siakuchitileni ngati waliyenche siwa mlekelela mbale kuchokela mumtima mwake.

Chapter 19

1Idachitika Yesu yapo wadamaliza mau yayo wadachoka Kugalilaya, ndi kupita mmalile mwa Yudea mchongolo mwa mchinje Jordani. 2Umyinji waukulu udamchata, ndi wa dalamicha kumeneko.3Mafarisayo adamjela, ndi kumuyesa, adamkambila, "bwa ndi uzene kwa mundu kumsiya mkazake pandande iliyonje?" 4Yesu wadayankha ndikukamba, "simudasome, iye wadakulengani mmayambo wadalenga wamuna ndi wakazi?"5Ndiposo wadakamba, pandande imene wamuna siwasiye atatewake ndaama wake ndi kugwilana ndi mkazane, ndi awili yawa sakale tupi limoji? 6Ndipo opande awilinjo, ila tupi limoji. Basi chija wachilunja Mulungu, mundu walionje wasada chisembanicha.7Adamkambila, "chopano ndande yanji Musa wadatiuza tijichocha hati ya talakandi kumsiya?" 8Wadakambila, "kolimba kwanu kwamitima Musa wadakuluhusuni kwa siya akuzi wanu, mambo choka mmayambo sidali chocho. 9Ndikukambilana, kuti walionje nyosiwamusiye mkazi wake, posa kale ndande yachigololo ndi wamuna waka kwata wamkazi wasiidwa wachita chigogolo."10Opuzila adamuuza Yesu, "ngati umuyalindi kwa wamuna wamkazi, opande bwino kukwata." 11Nampo Yesu wadakambila, "opande kila mundu wakoza kulandiza mayaluzo yaya, bali ndi kwaja tu avomelezedwa kulandila. 12Pandande alipo matoashi abadwa choka mmmba mwa amai wao. Ndi chocho kuli matoashi ndi wandu, ndi matoashi ya pajichita matoashi pandande ya ufumu wa kumwamba, wakanizila kulandila mayalzo yaya ndi wayalandile."13Ndipo wadapelekedwa baazi ya wana wangono ili waikile manja pamwamba pao ndi kupemba, nampo opuzila wake amakalipa. 14Bali Yesu wadakamba, "avomelezeni wana wangono, wala msidawakaniza kuja kwanga, pa ndande ufulu wa kumwamba ndi wawandu ngati amene. 15Ndipo wadaika manja yake pamwamba pao ndi kuchoka paja."16Penya mundu mmoji wadabwela kwa Yesu ndi kukamba, "mpuzisi, ndi chindu chaji chabwina chifunika ndichite ili ndi upeze kukala ndi umoyo osata?" 17Yesu wadamuuza, "ndichiyani undifusa dichindu chanji chabwino? Kuli mmoji tu wali wabwino, nambo ngata ufuna kupata umoyo, gwila malamulo ya Mulungu."18Yuja mundu wadamfuja, "ndi malamulo yati?" Yesu wadayankha, "usidapo, usidachita chigogolo, usidaba, usidakamba mtila, 19elemekeze atate wako nda amai wako, ndi mkonde jilani yako ngati umoyo wako."20Mundu yuja wadamkambila, "vindu vojevo ndavivela ndikuli kufuna chiyani?" 21Yesu wadakambila, "ngati wavela kala okamilika, pita, mapita kaguliche ulinavo, ndi wamikhe olumala, ndi siukale ndi ufulu kumwamba. Ndipo ubwele unichate." 22Nampo mnyamata yuja yapo wadayake layaje Yesu adamkambila, wadachoka kwa lisungu, pakuti wadali ndichuma chambili.23Yesu adakambila opuzila wake, "uzene ndikuuzani, ndikolimba kwa mundu wa chuma kulowa kuufumu wa Mulungu yoje yakozeka. 24Ndipo nikukambilani, ndi ulahisi kwa mgamiya kupita pakati pa jenje la sindano, kuposa pamundu olemela kulowa ku ufumu wa Mulungu."25Opuzila yapo adavela chocho, adadabwa sana ndi kukamba, "ndiyati kodi uyosi wa okoke?" 26Yesu wadapenya ndi kukamba, "kwa wandu limenelo sitikozekana, nambokwa Mulungu yoje yakozeka." 27Ndipo Petro wadamuyakha ndikumkambila, "penya, tasiya vonje ndikwalondola iwe, ndichindu chanji ichositipate?"28Yesu wadakambila, "uzene nikukambila, iye uyowanichata ine, pachibadwa chipya ndawi mwana wa Adamu yaposiwale pampando cha enzi cha ufulu waka namwe piya simukale pamwamba pa mipando kumi ndi viwili va enzi, kuwa ukumu maiko kumi ndi awili ya Israeli."29Kila mmoji wanu wasiyanyumba, kaka, dada, atate, amayi, wana, kapena munda pandande yajina langa, siwalandile mala mia ndi kulidhi umoyo osata. 30Nambo ambili ali oyamba saino, sakale otela, ndi aliotela sakale oyamba.

Chapter 20

1Chifuko cha ufuru wakumwamba ulingane ndi walindi mundo wauko umawa kupunda dele kuchofilila uchita nchito mmunda wake wa dhabihu. 2Pambuyo pakuti avemelezene ndiochita nchio kabili limoji pa siku limoji wada afume kutiapise mwande wake wazabibu.3Wadenitancho pambuyo pa ntawi zetatu ndiwa de awo odwa nchito ambili aimeima pakatikati po agulichila malonde. 4Wade akambila anyiimwe namweme pitani kumonde wa mzebibu ndi chilichonche chili chabwino sindikupacheni.5Wadapitancho pambuyo pa ntawi pita pambuyo pantawi tisa ndiswade chitancho chimwecho. 6Ntawi yenacho ntawi ya kumi na moja wadapita ndi kwapeze wine alibachilito wade akambila ndande yanji kwakala osachita nchito ntawi zonche. 7Adamkambila chifukwa palibe mvatu waliyenche walipache nchito wade akambilaaanyaimwe namwecho maputati kuno ne wa zabibu.8Ntawi yaujulo yapoidefika mwene mundo wa mizabibu wadamkambila aimilila atane ochita chito wapache melipilo yao payambila wotela mpaka ayamba. 9Yapo adabwela anyiwaja adapachidwa chitona kumi na moja pambuyo pamoja mmoji wao wadapachidwa ndelama. 10Yapo adabwela ochita nchito yamba adeyaizile kutisialandile za mbili kupunda achenjao nempo adalandila waliyonche ndelama imoji.11Pambuyo plandila naleme adamelanda ulile mvele mvundo. 12Adakamba anyiyawo afika kumetelo agwira chito ntawi imoji tu pogwira chito yao nampo watiikila nimoji ndiife habora katundu ntawi yaifuli ndi kupyedwa ndimoto.13Nampo mwene monde wadeuzakuti kwa mmoji wao bwanji rupa sindidachite kuipa bwanji silide langane ndiine ndolamo imoji? 14Landila chilichako ndi ujipata ndikukonde kwanga kwaapacho anyiyawa ogwira nchito chimoji moji ndiiwe.15Bwanji osatibwino kuchita chimene nachita pa chilichenga kapenya diso lako loipa chifukwa ine muntu wabwino. 16Mmwemo atela siwakale oyamba ndiayamba siwakale otela.17Yesu yapo wanakwela kupita kuyelusalemo wadaatenga ochasile wake kumi ndi awili pampepete ndimnjila wadeakambila. 18"Penyani fipata Kuyerusalemu ndimwane wa muntu siwa tilinidwe mmonja mkatimkati mwa mapadwi ndi olemba simlamole nyifa. 19Ndi simchoche kwa wantu achebedola kuachifa mwano kumfyopa nikumungaze nampo siku le katatu siwazuke."20Pambuyo maye wawane a Zebedayo adefika kwa Yesu ndi achikozi wadagwa miendu pachi ndi kumpemba chiudu kuchokile kwaiye. 21Yesu wade mfuche ufuru chiyani? wademkambila "lemule kuti anyiwa achiwane wanga anili akale mmoji janja lako la kwewe mmoji jalife lake la kmonjele paufuru wako."22Nambo Yesu wade yanka ndi kukamba, "siujiwa chimene upempe fiukoze kumwela chiko chimene sindi chimwele" adamkambila siti koze. 23Wade akambila chazene chiko chenge simchimwele nampo kukale janja langa la kumenjele ofisi chisu yanga kukupachani nampo kwa anyiwaja ato konjedwa ndi atate wange. 24Oyaruzidwa wake wena kumi yapo adavela ada dendeule kupunda ndi waje abale awili.25Nampo Yesu wadatana achinawene ndi kwa akambila mjiwe kuti achogoleli ajiko aovyeza ndi wakuru akuru wao kuvemeleza lamulo pamwamba pao. 26Nampo siidekale chimwecho kwa anyiimwe pambuyo pake waliyenche siwafune siwafune kukale wamkuru mkwati mwano ifunika wakale ogwira nchito wano. 27Ndiu ya siwakale oyamba mkafimwa au iyafunika wakale ogwera chito wanu. 28Ngati mmene mwana wa muntu siwadobwela kugwiridwira chito ikapande kugwira nchito ndikuchoche umoyo wake kukara mpurumuchi wa atwambili.29Ntawi ndiuchokela Kuyeriko wantu ambili ade mchata. 30Ndi wade aone osapenya awili akala pampepete panjila yapo adovera kuti Yeu wali mkupita ado kweza mau ndikukamba wamkuru mwana wa Daudi uti uonele lisungu. 31Nampo wantu ambili ada akanize ndi kwakambila kaleni kachete ata chimwecho anyaiwo adekweza mau kupunda ndi kukama wamkuru mwanewa Daudi utiavela lisungu.32Pambuyo pake ayesu wadaimondikwa atana kwa afuche mufune ndikuchisile ni chiyani. 33Adamkambila "kuti wamkuru maso yatu yapeza kupenya." 34Pambuyo Yesu wadepeza lisungu wade pambale maso yao ntawi yomweyo atapeza kupenya ndi kumchota.

Chapter 21

1Yesu ndi opunzila wake adepita pafupi ndi ku Yerusalemu ndi kupita mpakana ku Bethfage, mwa pili la Mizeituni ndipo Yesu adawatuma opunzila awili. 2Kwakambila, "pitani kuchinjhijhi chochatila, ndipo mara kamojhi simumpheze punda wamangidwa pajha ndi mwana wa punda pamojhi ndi iye. amasulani ndi kunipelekla ine. 3Ikakala mundhu waliyenche akakukambilani chalichonche kukhuza chimenechosimkambe, ambuye awafuna. Ndi mundhu mmeneyo mara kamojhi siwampeleke udendo mbwele pamoji ndi anyiiwo."4Chito ili lidachokela ndi lijha lidakambidwa kupitila kwa olosa nditu likwanilidwa. Adakambila, 5"akambileni anamwali Akusayuni, penyani fumu yako ikjha kwenu, ojhichicha ndi walikukwela punda, ndi mwana wa punda wa mmuna, mwana wa punda wateta."6Ndipo opunzila adachoka ndi kuchita ngati Yesu umu adawatumila. 7Adampeleka pundandi mwana wa punda, ndi kuyala nchalu zao mawamba mwanyiiwo, ndipo Yesu wadakala pajha. 8Ambili mwa gulu adayala nchalu zao. Mnjila ndi wana adadula nthawi kuchoka mumitengo ndi kuyala mnjila.9Gulu lidamchogolela Yesu ndi anyiwajha adamchata adakuza mau ndi kunena, "Hosana mwana wa Daudi! Ndi wa Mwawi wa kujha kwa jina la Ambuye. Hosana kumwamba kupitilila! 10Yesu yapowadafika ku Yerusalemu mujhi wonche udajhijhimuka ndi kunena, 'uyu ndi yani?' 11Gulu lidayankha, uyu ndi Yesu olosa, kuchoka Kunazarethi ya Galilaya."12Ndipo Yesu wadalowa muhekalu la Mulungu, adawatamangichila kubwal wonche yawo amagula ndi kugulicha muhekalu. Pamurepo wadeng'anamula meza yawo awasindhishana ndelama ndi mipando yawogulicha nghunde. 13Adakambila, "yalembedwa" nyumba yanga siitanidwe nyumba ya maphembelo, nampho anyiimwwe mwaichita jhenje la akuba. 14Ndipo osapanya ndi opunduke adamjhela muhekaluni naye adalamicha.15Nampho nyengo wakulu wakulu wanchembe ndi olemba yapoadaona vodabivicha wadevichita ndeyapo adavela wana amenyepokoso muhekalu kunena, "Hosana kwa mwana wa Daudi" adagwilidwa ndi mbhwayi. 16Adamkambila, "wavela chija chikambidwa ndi yawa wandhu?" Yesu akambila, "yetu! Nampho simdachitepo kuwelenga kuchokela kumilomo kwa wana ateta oyamwa muli ndi kutogoza kokwanila? 17Ndipo Yesu adawasiya ndi kupita kubwalo la mujhi mwa Bethania ndi kugona kumweko."18Umawa yapo wamabwela munjhini wa dali wali njala. 19Adaona mtengo mphepete mwa mseo. Adamchata, nampho siwadapeze chindhu nimwamba mwake ikapanda machamba, adaukambila kusadekala ndi vipacho kwa kwajwe nyengo zonche ndi mmemo mtengo ujha udauma.20Opunzila yapoadaona, adadebwa ndi kunena, "yakala bwanji mtengo wauma mara kamojhi?" 21Yesu wadayankha kwambila, "zene ndikukambilani, ngati mkakala ndi chikulupi popande chiphwe mbezi simchita chijha chidachitika kwa uwo mtengo pe, nampho simlikambile mpakana pili, litengedwe ndi likataidwe mnyanja nai siichitike. 22Chalichonche simphembe kwa kupemphela ndi ukumkulupalila simlandile.23Yesu yapo wadafika mhekalu wakula kulu anchembe ndi midala ya wanhu adamjhela nyengo wadali mkuyaluza ndi kumfuncha, "kwa malamulo yati uchita nghani izi? Ndi yani wakupacha malamulo yaya? 24Yesu wadayankha ndi kwakumbila, "ndiine nanencho sinikufuncheni fujho limojhi. Ngati sinikambile nanencho mmwemo sinikukambileni kwa malamulo yati nichita vichito vimenevyo."25Ubatizi wa Yohana - udachoka kti kumwamba kapena kwa wandhu? Ada chimikizana achinawene, kunena, tikanena udachoka kumwamba siatikambile kwa ndande chiyani simdakulupalile? 26Nampho tikanena udachoka kwa wandhu, taopa agulu kwa ndande wonche aupenya Yohana ngati olosa. 27Ndipo adamuyankha Yesu kunena, "sitijhiwa" adakambilancho ingakale ine sinikukambilani kwa malamulo yati nichita vichito ivi.28Nampho naniza chiyani? Mundhu uyo wali ndi wana awili wadapita kwa mmojhi kumkambila, mwanawanga mapita ukachite, nchito mmunda mwa mpelesa. 29Lelo. Mwana wadayankha kunena, sinipita nampho pambuyo wadang'anamuka maganizo yake ndikupita. 30Ndi mundhu yujha wadepita kwa mwana wa kawili kukamba chindhu chimwechijha. Mwana mmeneyo wadayankha kunena sinpite atate nampho siwadapite.31Yuti pakati pa wana awili wadachita chifuno cha atate wake? Adanena mwana woyamba. Yesu adakambila cha zene nikukambilani osogecha chume ndi achigololo sialowe mu ufumu wa mulungu muvuli anyiimwe kulowa. 32Pakuti Yohana wadajha kwa anyiimwe kwa njila iyo yotambeluka nampho simdamkulupalil, nyengo osogecha chuma ndi achigololo adamkulupalila. Namwecho, yapomdaona limenelo lichitika simdakoze kulapa kuti pambuyo mukulupalile.33Vechelani chifanizo chena. Kudali ndi mundhu, mundhu mwene malo ya kulu ya nthakha. Wadavyala mipelesa wadajiikila seli wdakovya chindhu cha kkamulila divai, wadamanga mtoonji wa mlonda, ndi kulibwelekecha kwa osunga mpelesa, ndipo adapita mmayiko. 34Nyengo ya mavuno ya mipelesa yapo yadawandikila adawatuma akumojhi ya atumiki kwa olima wa mipelesa kutenga mipelesa yake.35Nampho alimi wa mpelesa adawatenga atumiki wake, ada mbula mmojhi, kumpha mwena, ndi adamula mmojhi kwa mwala. 36Kwa mara yena oyimilila adatuma atumiki wena, ambili kupitilia oyambe, nampho olima wa mpelese adachitila mmwemujha. 37Pambuyo papamenepo atate wajha adamtuma kwa anyiiwo mwana wake kunena, "siamlemekeze mwana wanga."38Nampho olima wa mpelese yapoadamwona mnyamata yujha adakambilana , "uyu ndi osidwila majhani timphendi tiimilile yosiidwa." 39Ndipo adamtenga, kumtaya kubwalo la munda wa mpelesa kumpha.40Bwanji mwene oimilila wa munda yaposiwaje, siwachite chiyani ohima wa mipelese? 41Adamkambila, "siwawanange yawo wandhu oyipa mwanjila ya mbwayi kupunda ndi pamwepo kuwapacha munda wa mpelesa kwa olima wana wa mpelesa wandhu yawo siwalipe kwa chifuko cha mpelesa yaposiupye."42Yesu adakambila, "simdawelenge mmalembo, mwalo uwo adaukana omanga wa kala mwala wa ukulu wa chilili. Ililachokea kwa ambye, silidabwiche pamoso patu?"43Mmwemo ni kukambilani ufumu wa Mulunu siutengedwe kuchoka kwa inyimwe ndi kupachidwa jhiko lisamalle vipacho vake. 44Waliyenche siwagwe mwamba mwa mwala umeneo siwadulidwe vigawo vigawo. Nampho kwa waliyenche uyosilimgwele, silimpele.45Wakulu wakulu anchembe ndi Mafarisayo yapo adavela vifanifani vake adaona kulti wakambilila anyiiwo. 46Nampho yapo amafuna kutambasula manjhe kumwake kwaiiye, adawopa magulu, kwandande wandhu adampenya ngati olose.

Chapter 22

1Yesu wadakamba noncho kwa chifanizo kuti, 2"ufumu wa kumwamba ufanana ndi mfumu wa dakonja pwando la ukwati wa mwana wake. 3Wadaatuma atumiki wakeyao atanidwa kupwado la ukwati nampho sadafike."4Mfumu wadatuma atumiki wina kuti, "akambilani onche atanidwa, penyani nakonja chakudya cha mate ndi wana ang'ombe onona apedwa ndi vinthu vonche vatokonjeka, majani kupwando la ukwati."5Nampho wanthu otanidwao sadaone ngati chinthu cha mate kutanidwako akumoji adabwelela mminda mwao ndi wina adabwelela mmabizines yao. 6Wina adaakila atumiki amfumu ndi kuapanga mwano ndi kuapa. 7Nampho mfumu wadakwia ndikuatuma asiriali wake ndi adaapa akupao ndi kupyeleza muji wao ndi moto.8Nde wadaakambila atumiki wake, "ukwati watokonjeka kama otanidwa okana kuja. 9Kwa icho pitani mmiso nkhano ya njila ya ikulu kupwando la ukwati. 10atumika adapita njila ya ikulu ndi kuatana wanthu alionche adaona, abwino ndi oipa, kwa icho nyumba ya ukati idajala alendo."11Nampho mfumu yapo wadalowa ndi kuapenya alendo wadamuona munthu mmoji siwadavale nchalu ya ukwati. 12Mfumu wadamfuncha abwenji mwafika bwanji mnyumba muno popande nchalu ya ukwati? Munthuyo siwayankhe kanthu.13Ndipo mfumu wadakambila atumiki wake, "mmangeni munthuyu manja ndi muyendo ndi muntaye kubwalo kumdima, kumene sikukale chililo ndi kugaya mano. 14pakuti atanidwa ambili asankhidwa ochepa."15Ndipo afarisayo adachoka ndi kupanga mtundu wa kumgwila Yesu mmau yake mwene. 16Ndipo adatuma opunzila wao pamoji ndi ma herode, ndi adamkambila Yesu "Mpuzisi" tijiwa kuti iwe ndi munthu wa zene, ndi kuti uyaluza mafuno ya Mulngu mu uzene siuvechela va wanthu ndi siumkondelela munthu. 17Kwa icho tikambile uganizila chiyani chiyani? Bwa nizoona kuchocha sonkho kwa Kaisari kapena noto?18Yesu wadajiwa kuipa kwao ndi wadaakambila, ndande chiyani mniyesa anyiimwe opande chilungamo. 19nilangizeni ndarama iyo mchochela sonkho nde adampelekela dinari.20Yesuwadaafuncha mphumi ndi jina ili ndi va yani? 21Adamuyankha "va kaisari" ndipo Yesu wadaakambila mpacheni Kaisari ivo vili vake ndi va Mulungu mpacheni Mulungu. 22Yapo adavela chimwecho adadabwa, adamsia ndi kuchokapo.23Siku limenelo Masadukayo akumoji adaja kwa Yesu anyiwaja akamba kuti palibe kuyushidwa kwa wanthu akufa, ndi kumfuncha. 24Apunzisi Musa wadakamba ikakala munthu wafa popande kubala wana m'bale wake wamkwate wamkaziyo ndi kumpatila mwana m'bale wake.25Adalipo abale asanondi awili saba oyamba wadakwata ndi kumwalila popanda wana wadamsiila m'bale wake wamkazi. 26Ndipo m'bale wake wa kawili naye wadachita chimwecho, ingakale wakatatu, idali chimwecho mbaka yuja wa saba. 27Pambuyo pake yapo adachita chimwecho onche adamkwatila. 28Chapano pa chizyukililo wamkaziyo siwakale wa yanipa abale sabao? Ndande onche adamkwatila.29Nampho Yesu wadaayankha ndi kuakambila, mlakwila ndande simjiwa malembo ndi mphavu za Mungu. 30Ndande pa chizyukililo wanthu saakwata wala kukwatiwa, pambuyo pake akala ngati angelo kumwambako .31Nampho kukuza chizyukililo cha akufa, simdasome chija Mulungu wadachikamba kwanu kuti, 32ine ndi Mulungu wa Ibrahimu, Mulungu wa Isaka, ndi Mulungu wa Yakobo? Mulungu asati Mulungu wa akufa nampho Mulungu wa yao alimoyo. 33Msonkhano yapo adavela yaya adadabwisidwa ndi mayaluzo nyake.34Nampho Mafarisayo yapo adavela kuti Yesu wakalicha kachete asadukayo, adajikusa achinawene pamoji. 35Mmoji wao wamatauko wadamfuncha Yesu ino muyesa 36"apuzisi ndi lamulo liti lalikulu kupunda zina zonche kumatauko?"37Yesu wadamuyankha, "mkonde Ambuye Mulungu kwa mtima wako onche ndi njelu zako zonche. 38Iyi nde lamulo la likulu ndi yoyamba.39Yakawili ifanana ndi imeneyo kuti umkonda wapafupi wako ngati umo ujikonda umwene. 40Matauko yonche ndi olosa akulupalila matauko yaya yawili."41Mafarisayo akali ajikusa pamoji, Yesu wadaafuncha funcho. 42Wadakamba muganiza chiyani kwa Kriso? iye ndi mwana wa yani? "Adamuyankha ndi mwana wa Daudi."43Yesu wadaayankha, kwa mtundu wanji Daudi mwa mzimu wamtana ambuye ndi wakamba. 44Mulungu wadamkambila Ambuye wanga "kala janja la kwene mbaka yaposiniachite oipa wako aikidwe panchi ya myendo yako?"45Ngati Daudi wamtana Kristo Ambuye wakala bwanji mwana wake? 46Palije uyo wadamuyankha mauncho ndi palibe uyo wadayesakumfuncha mafuncho chiyambile siku lija ndi kuendekela.

Chapter 23

1Pambuyo wadakambana ndi msonkhano wa wanthu ndi opuzila wake, wadakamba, 2"olemba ndi Afarisayo akalila mpando wa Musa. 3Kwa icho chalichonche icho waalamulila kuchita, chitani uku nampho msdaviesa vichito vao kwa chifuko anyaio afuna vinthu ivo saavichita."4Kwa chazene anyiyao amanga makatundu yolemela, ene yolimba kuyasenchela ndi pina kumaasechecha wanthu mmapewa mwao, nampho anyaio achinawene saasendeza ata chala kuinyakula. 5Vichito vao vonche, avichita kuti apenyedwe ndi wanthu kwa ndande anyaio aongezela mabokosi yao ndi kuongezela ukulu wa mapindo ya vovala vao.6Anyaio akondeleza kukala pamalo ya olemela katika sherehe ndi akati pa mipando ya ulemu mkati mwa sinagogi, 7ndi kulonjeledwa ka ulemu pamalo pa msika, ndi kutanidwa "mapuzisi" ndi wanthu.8Nampho anyaimwe simfunika kutanidwa "mapuzisi" pakuti mulinayo puzisi mmoji, ndi anyaimwe mwaonche ni mabale. 9Msadamtana munthuwaliyonche pano pajhiko kuti atate wanu, pakuti mulinao atate wanu amojhi nao ali kumwamba. 10Wala msadajha kutanidwa "mapuzisi" pakuti mulinao apuzisi amojhi yaani Kristo.11Ingakale uyo wali wamkulu pakati panu siwakale wanchito wanu. 12Waliyonche wajhikweza siwachichidwe, ndi waliyonche uyo wajhichicha siwakwezwedwe.13Nampho ole wanu olemba ndi Afarisayo, anafiki! Mwaamangila wanthu ufumu wa kumwamba. Namwe simukoza kuulowa, ndi kwalamula anyiyao alowa kuchita n'chimwecho. 14(Gwililila: Mzele 14 siuonekane katika nakala za bwino za kale. Pamal pa nakala ziongezeka mzele pamalo pa mzele wa 12. Mzele wa 14 ole wanu olemba ndi Afarisayo anafiki! Pakuti mwaameza ofedwa''). 15Ole wanu olemba ndi Afarisayo anafiki! Muyomboka mchijha mwa nyana ndi kufika ndi kumchita munthu mmojhi wayaamini yajha muyayaluza, ndi yapo wakala ngati anyaimwe mwa achinawene umo muli.16Ole wanu ochongoza osapenye, anyaimwe mkambao, waliyonche walumbila kwa hekalu opande kanthu. Nampho uyo walumbila kwa dhahabu ya hekalu, wamangidwa kwa chilanga chake. 17Anyaimwe osapenye apumbalu, chiti chachikulu kupitilia chinjake,dhahabu kapena hekalu, ilo laika wakfu dhahabu kwa Mulungu?18Ndi waliyonche walumbila kwa madhabahu, opande kanthu, nampho uyo walumbila kwa nchembe iyo ili pamwamba pake, wamangidwa kwa chianga chake. 19Anyaimwe wanthu osapenye, chiti chachikulu kupitilila chinjake, nchembe kapena madhabahu, iyo iika wakfu nchembe izozichochedwa kwa Mulungu?20Kwa icho iye walumbila kwa madhabahu walumbila kwa chimwecho ndi kwa vinthu vonche ivo vili pamwama pake. 21Nae wakumbila kwa hekalu, walumbila kwa limenelo ndi kwaiye wakalayo mkati mwake. 22Ndi iye walumbila kwa kumwamba, walumbila kwa mpando wa enzi w Mulungu ndi waiye wakala pamwamba pake.23Ole wan olemba ndi Afarisayo, anafiki, pakuti mulipa zaka kwa bizali,mnaanaa ndi mchicha, nampho musiya vinthu volemela va sheia, haki, rehema ndi imani nampho yaya mfunika kukhala mwayachita, ndi osati kuyasiya popande kuyachita. 24Anyaimwa mwachogoza osapenye, namw mucheza chidudu chaching'ono nampho mukoza kummeza ngama!25Ole wanu olemba ndi Afarisayo, anafiki! Pakuti muchuka kubwalo kwa vikome ndi kubwao kwa mbale, nampho mati mwajhala dhuluma ndi klepela kukhala ndi kiasi. 26Anyaimwe Afarisayo osapenye, chukani poyamba mkati mwa chikombe ndi mkati mwa m'bale, bendekala kubwalo nalo likale labwino.27Ole wanu olemba ndi Afarisayo, anafiki! Pakuti mulingana ndi mainja, yayoyapakidwa chokaa, yaya yali kubwalo yaonekana ya bwino, nampho kwamkati yajhala vifupa va akufa ndi kila chinthu icho chili chichafu. 28Chimwecho nde icho, namwe kwa kubwalo muonekana muli ndi haki pachogolo pa wanthu nampho kwa mkati mwajhala unafiki ndi unkhungu.29Ole au olemba ndi Afarisayo, anafiki! Pakuti mwamanga mainja ya olosa ndi kuyapamba mainja ya anyiyao ali ndi haki. 30Anyaimwe mukamba, ngati tidakhala siku za achaa atate watu, sitidakhala tashiliki pamojhi nao kuumwaa mwazi wa olosa. 31Kwa chimwecho mwajhishuhudia mwa achinawene kuti anyaimwe ndi wana wa anyiyao wadaapa olosa.32Tena anyaimwe mukamilisha kujhaza malo yayo yafunika zambi ya atate wanu. 33Anyaimwe njoka, wna wa vipilibao, kwa mateyanji simulikane lamulo la kujhehanamu?34Kwa chimwecho, penya, naatuma kwanu olosa, wanthu aulemu, ndi olemba, wena wao simwaape kwa kuwalindilila ndi wina wao simwatyape mkati mwa masinagogi yanu ndi kuwatopola kuchokela mujhi umojhi mbaka unjake. 35Mayankho ndi kuti pamwamba panu sipachokele mwazi onche wa anyiyao ali ndi haki uo wataika pajhiko, kuyambila mwazi wa Habili mwene haki maka kwa mwazi wa Zakaria mwana barakia, uyo mudampha pakati pa poela ndi madhabahu. 36Zene, nikakukambilani, mambo yaya yonche siyapate ubazi uno.37Yerusalemu, Yerusalemu iwe waipha olosa ndi kuwabula myala anyiwaja anyiyao atumidwa kwako! Mala kangati naukusanyani wana wako pamojhi ngati nkhuku mujha yayaakusanyila wana wake panchi pa mapapiko yake, nampho siudavomele? 38Penya nyumba yako yakhala ndi chisoni. 39Yani wakukambila, kuyambila chipano ndi kuendekela siuniona , mbaka yapo siukambe, wabarikidwa iye wakujha kwa jhina la Ambuye.

Chapter 24

1Yesu wadachoka ndikupita zake opuzila wake adamuendela ndikumlangiza manyumba ya hekalu. 2Nampho wadayankha ndikwaakambila, "bwa simuyaona mambo yaya yonche? Kweli nikukambilani palibe mwala siliale pamwamba paliwa bila kubomoka."3Ndi yapowadakala papili pa mizeituni, opuzila wake adamuendela kwa furaha ndikukamba, "tikambileni vintu sivichokele chakanji chintu chanji sichikale dalili ya kuja kwako ndi potela pa jiko?" 4Yesu wadayanka ndikakambila, mkale makini kuti siwadaja muntu kuwapotosha. 5Pakuti ambili siaje kwa jina langa siakambe, inende Kristo ndi siaptoshe ambili.6Simvele ukondo ndi nkhani za nkondo penyani msidaja kukala ndi mantamanta, pakuti vinthu visiyafunika kuchokela, nampho ujaotela siukale ukali. 7Pakuti jiko siliinuke dhiki yalina, ndi uflume dhidi ya uflume sikukale ndinjala ndi kutentemela ntaka katika sehemu zambili zambili. 8Nampho vinthu ivi vonche ndi mwazo wa uchungu wa kujimasula.9Ndiyapo siachoche kwa chifuko cha mayeso ndi kwaipa simuipidwe ndi jiko lonche kwa chifuko cha jimalanga. 10Ndiyapo ambili siajikowale ndi ndi kusalitiana ndi siaipilane achinawene kwa achinawene. 11Manabii ambili amtila siachokele ndi kwamyenga ambili.12Kwa chifuo uovu siuongezeke, chikondi cha ambili sichipole. 13Nampho uyo siwavumilie mpaka potel siwakoledwe. 14Li injili ya uflume siatangaze jiko laphumbu ngati ushuhuda wa taifa yonche ni yapo uja uflume otela siuje.15Kwa chimwecho, yaposimpenye simuipidwe nikuwanangika, ilo likambidwa ndi nabii Daniel laima pamalo pa utukufu (uyosiwasome ndi ufahamu). 16Ndiyapo alikuyuda atamangile kumapili. 17Ndi yuja walikumwamba yapaa la nyumba siwadankoza kuchika panchi kutenga chinthu chalichonche mkati mwa nyumba yake. 18Nayo walikumunda siwadabwela kutenga uchalu zake.19NAmpho ole wao ambao alindi wana ndi waja ayamwicha katika siku zimene. 20Pemphani kuti kutamanga kwanu sikudakala nyeno ya mphepo wala siku ya kusali. 21Pakuti sikukale ndi taabu yaikulu, ambayo siidawahi kukalapo tangu kubadwa kwa jiko hadi chipano wala siikalanicho. 22Ngati siku zimene sizifupichidwe palibe ambae siwaokoke. Nampho kw chifuko ya uteule, siku zimene siazifupiche.23Ila idali munthu walienche siakukambileni penyani Kristo waliyapa! Au, "Kristo walikuja" msiyaamini mau yake. 24Pakuti makristo amtila ndi manabii amtila siaje ndi wateule. 25Penyani, "nikutahalishani kabla ya vinthu ivi kuchokela."26Kwa chimecho ikakala siakambiidwe, "Kristo waliko kujangwani, Au penyani, wali mkati mwa nyumba msidayaamini mau yameneyo. 27Ngati muja mphambe yapoimulika kuchokela kumashariki ndikuangaza hadi magharibi ndiumo siikalile kuja kwa mwana wa Adamu. 28Paliponche ulipo mzoga, kumene ndetai akusanyikapo."29Nampho mara pambuyo padhiki yaikulu sikuzija, jua silikale mdima, mwezi siuchocha dangalila lake, ntondwa sizigwe kuchoka kumwamba ndi mphavu za kumwamba sizitingizike.30Ndeyapo ishara ya mwana wa Adamu siionekane kumwamba, ndi makabila yonche yajiko siaomboleze, siamwaone mwana wa Adamu niwaja kuchokela mmitambo ya kumwamba kwa mphavu ndi utukufu wa ukulu. 31Siatume malaika wake kwa sauti yaikulu ya tarumbeta inao siakusanyie pamoji niwateule wake kuchoka pande zinai zajiko, potela mmoji wa kumwamba hadi mwina.32Jiyaluzeni somo kuchokana ndi mtengo mtengo mitengo, mara tuntawi yaposipuke ndikuchocha machamba simujiwe kuti mwavu wakalibia. 33Chimwecho, yaposimuone vinthu ivi vonche, mfunika kujiwa kuti, wasendele sendelela ndi chicheko.34Kweli ndikukambilani kizazi ichi siupita hadi vinthu vonche ivisivikale vachokela. 35Kumwamba ndi panchi sipapite, nampho mau yanga siyapita kamwe.36Nampho kuhusu siku lija nda ntawi palibe muntu siwaijiwe, ata malaika akumwamb, wala mwana, ila ambuye okope. 37Ngati muja idali katika siku za Nuhu, ndiumo sikalile kuja kwa mwana wa Adamu. 38Pakuti siku zimenezo kabla ya gharika wantu adalinaadya ndiumwa, akwata ndikukwatiwa hadi siku lija ambayo Nuhu wadalowa katika safina. 39Ndi siadajiwe chinthu chalichonche hadi gharika yapoidaja ndi kwakokola onche, ndechimwecho umosidakalile kuja kwa mwana wa Adamu.40Ndeyapo wantu awili siakale nasaga mmoji siwatengendwe ndimmoji siwasiidwe mmbuyo. 41Wachikazi awili siakale kumunda pamoji mmoji siwatengedwe ndi mmoji siwasiidwe. 42Kwachimwecho kalani maso kwa chifuko simjiwa siku lanj ambalo siaje ambuye wanu.43Nampho mjiwe kuti, ikakala ambuye wene nyumba angadajiwa ndi ntawi yanji mnungu siwaje, wadakesha ndi siwadakalamula nyumba yake kuloweledwa. 44Kwachimwecho, mfunika kukala tayali, pakuti Mwana wa Adamu siwje ntawi iyosimuikulupalila.45Chimwecho ndiyani walioaminika, mtumwa walininjelu, ambayo ambye wake ampacha malamulo pamwamba katika nyumba yake, ili wapachidwe chakudya kwa nyengo yabwino. 46Wabarikiwa mtumiki mmeneyo, ambayo ambuye waka siampeze niwachita chimwecho nengo niwaja. 47Kweli nikukambilani kuti siamuike pamwamba pa kila chinthu chili chake.48Nampho ngati mtumwa muovu wakakamba mmiima mwake, Ambuye wanga wachedwa. 49Ndi wadayamba kwaabula watumiki wake ndi wadadya ndikumwa volejela. 50Ambuye wa mtumwa mmeneyo siwaje katik siku iyo saikulupalila, ndi katia ambayo siwaijiwa. 51Ambuye wake siamdule vipande viwili ndikumuika katika nafasi imoji sawa ndi wanaik, ambapo sikukale ndi chililo ndikusangamano.

Chapter 25

1Ndeyapo ufumu wa kumwamba ulinganishidwa ni wachikaza kumi atenga taa zao nikuchoka kupita kumlandila omange ukwati. 2Asano akumoji wao apumbavu ni asano wina adali oelewa. 3Wanawali apumbavu yapo adatenga taa zao, siadatenge mafuta yaliyonche. 4Ila wanawali oelewa adatenga vyombo vili ni mafuta ni taa zao.5Chapano muda bwana arusi wachedwa kufika, onche adabanidwa ni litulo ni adagone. 6Nampho muda wa usiku wa pakati kudali ni kelele, "penya bwana arusi chokani kubwalo mkamlandile."7Ndeyapo wanawali onche adauka ni kuwasha taa zao. 8Anyiwaja apumbavu wadakambila anyiwaja ojiwa, "mtupache malo ya mafuta yanu kwa ndonde taa zanu zitodima. 9Nampho anyiwaja ojiwa wadayankha ni kwakambila pakuti siyatitosha if ni anyiimwe, badala yake pitani kwa ogulicha mkagule kiasi kwa ajili yanu."10Muda apita kumeneko kugula, bwana harusi wadafika ni onche adali tayari adapita nae kusherehe ya ukati ni chicheko chidachekedwa. 11Baadae anyiwaja wanawali wina nao adafika ni kukamba, Ambuye, Ambue, mtuchakulile. 12Nampho wadayankha ni kukamba, "zene nikukambilani, ine simikujiwani." 13Kwa icho penyani, pakuti simujiwe siku wala nthawi.14Pakuti ni sawa ni munthu yapo wadafune kuchoka kupita jiko lina. Wadatana otumika wake ni kwa minkha chuma chake. 15Mmoji wao wadampacha talanta zisano, mwina wadampacha ziwili, ni yuja mwina wadampacha talanta imoji. Kila mmoji wadalandila kiasi kuchokana ni uwezo wake, ni yuja munthu wadachoa ni kupita zake. 16Chisango yuja wadalandila talanta zisano, wadapita kuikiza, ni kubalicha talanta zina zisano.17Chimwecho yuja wdalandila talanta ziwili, wadabalicha zina ziwili. 18Nampho otumidwa wadalandila talanta imoji, wadapita zake wadakumba jenje panchi panthaka ni kuibisa ndalama ya mfumu wake.19Ni baada ya muda wa utali, bwana wa boi achameneo wadabwela ni kukonja mahesabu nianyiio. 20Yuja boi wadalandila senti zisano wadaja ni kupeleka sent zina zisano, wadakamba, bwana udamininka sent zisano. Penya napata faida ya sent zina zisano. 21Bwana wake wadamkambila, chabwino boi wa bwino ni okulupalilika! Wakala okulupalilika kwa vinthu vaving'ono. Nikupache kukala juu ya vinthu vambili. Lowa katika raha ya Bwana wako.22Boi wadalandila sent ziwili wadaja nikukamba, Bwana udanipache sent ziwili. Penya, napata faida ya senti zina ziwili. 23Bwana wake wadamkambila, "chabwino, boi wa bwino ni okulupalilika! Wakala okulupalilika kwa vinthu vochepa. Nikupache malamulo juu ya vinthu vambili lowa katika chisangalalo cha bwana wako."24Baadae boi wadalandila senti imoji wadaja ni kukamba, 'Bwana, mjiwa kuti iwe ni munthu ong'ang'ala. Ukucha pamalo yapo udavyale, ni uvuna pamalo yapo udaganizile.' 25Ine midaopa, midapita zanga kuibisa senti yako katika doti. Penya ilipo pano ija ili yako.26Nampho Bwana wake wadayankha ni kukamba, iwe boi oipa ni mzembe, udajiwa kuti nikucha pamal ambapo midavyale ni kuvua pamalo ambapo nidaganizile. 27Kwa icho idafunika kwa pacha ndalma yanga wanthu abalicho, ni muda wanga obwela nidailandila yanga ija pamoji ni yobala.28Kwa icho mlandeni imeneyo senti ni mpacheni yuja boi wali ni senti kumi. 29Kila munthu walinacho, waongezedwe yambili ata kwa kumzidishia kupunda. Nampho kwa waliyonche walija chinthu, ata icho walinacho siwalandidwe. 30Mponyeni kubwalo mmene boi siwafai, uko kukale ni malilo ni kupela mno.31Muda mpulumusi yaposiwaje katika ufulu wake, ni angelo onche pamoji ni uje, nde yapo wakale pamwamba pa mpando wake wa ufulu. 32Maiko yonche yakusanyane pachogolo pake naye siwagawe wanhu ngati umo owesa wazigawila mbelele ni m,buzi. 33Waziike mbelele janja lake la kwene, ila buzi waziike janja la kumanjele.34Pambuyo mfumu siwakambile anyiwaja al janja lake la kwene, majani mwajalisidwa ni Baba wanga, kalani ni ufumu waikidwa chanu tangu kuikidwa chizindikilo cha jiko. 35Pakuti nidali ni njala ni mdanipacha chakujan nidali mlendo ni mdanikaribsha. Nida maliseche ni mdaniveka nchalu, nidali odwala ni mdanipenyelela. 36Nidali maliseche ni mdanive ka nchalu, nidali odwala ni mdanipenyelela. Nidali kndende ni mdanifikila.37Ndeyapo alini haki siamuyankhe ni kumkambila, Ambuye liti tidakuonani muli ni njala, nikukujechani? Au muli ni lujoni kukupachani maji? 38Niliti tidakuonani muli mlendo, ni lidakukaribichani? Au muli maliseche ni tidakuwekani nchalu? 39Ni liti tida kuonani muli odwala, au katika kundende ni tidakujelani? 40Ni mfumu siwakuyankheni ni kukukambilani, zene nikukambilani, icho mwachita yapa kwa mmoji wachabale wanga wang'ona, mdanichtila ine.41Ndeyapo wakukambileni anyiyao ali janja lake la kumanjele, chokani kwanga, mwalanidwa, pitani katika moto wa milele waandalidwa chifuko cha satana ni angelo wake. 42Chifuko nidali n njala mdanipache cha kuje. Nidali ni lujo nampo mdanipache maji. 43Nidali mlendo nampho mdanikaribishe, nili maliseche nampho mdanipache nchalu; Nili odwala ni nile kundende nampho mdanipenyelele.44Ndeyapo anyiio nao amuyankhe ni kukamba, Ambye, liti tidakunani mli ni njala, au muli ni lujo, au muli mlendo, au muli malisech, au muli odwala, au muli kundende ndi tidakutumikileni? 45Nampho wakuyankheni ni kukamba, zene nikukambilani, chija ambacho mdachite kwa mmoji wa anyiyawa wana, mdanichitile ine. 46"Anyiyawa apite katika kulangidwa kwa moja kwa moja ila alini haki katika umoyo wa muyaya."

Chapter 26

1Nzenga Yesu wadamaliza kukamba mau yonche ya wadakambila opuzila wake. 2"mujiwa kuti baada ya siku ziwili sikunkale ni sikukuu ya Pasaka, ni mwana wa mwanadamu siwanchochedwe ili waburidwe."3Pambuyo pake wakulu-akulu wa makuhani ni midala ni wanthu adamphozana pamoji kupitila pamalo pa kuhani wa mkulu, uyo wamatanidwa Kayafa. 4Kwa pamoji adapanga njelu ya kumgwila Yesu kwa kujibisa ni kumpa. 5Pakuti adakamba, "isidachitidwe nyengo ya sikukuu, ili isidaja kuzuka kuipidwa mkati mwa wanthu."6Nyengo Yesu waedali Bethania mkati mwa pankoma pa Simoni mkoma. 7Yapo wadajinyoosha pameza, wamkati mmoji wadamchota iye uku watenga mkebe wa alabasta iyoidali ni mafuta yali ni thamani yakikulu, ni wadayatililila pamwamba pa mutu wake. 8Nampo opuzila wake yapoadaona na vichito vimene va adaipila ni kukamba, "chiani ndande ya hasala? 9Yaya yadakamkoza kugulichidwa kwa kiasi cha chikulu ni kuninkhidwa osauka."10Nampho Yesu wadajiwa limenelo, wadakambila, "ndande chiyani kumchaucha wamkazi uyu? Pakuti wachita chinthu cha bwino kwanga, 11Masikini mulinao siku zzonche, nampho simnkala pamoji ni ine nthawi zonche.12Ndande yapo wtiilila mafuta yaya pamwamba pa nthupi langa, wadachita mchimwecho ndande ya kulikidwa kwanga. 13Uzene nikukambilani, paliponche mau ili yaposi kambilidwe pakati pajikho lonche chichito ichowachichita uyu wamkazi, ni siikale niikambidwa ndande lamau la kukumbukidwa.14Ndipo mmoji wa anyiwaja kumi na ni awili, uyowatanidwa Yuda Iskariote, wadapita kwa wakulu anchembe. 15Ni kukamba, "Simunininkhe chiyani kumuukila?" Adampipila Yuda vipande thelathini va hela. 16Tangu nyengo imeneyo wadafunafuna nafasi ya kumuukila.17Ata siku yo yamba ya mikate iyosidantilidwe sumu, wanafunzi adamchota Yesu ni kukamba, "kuti ufuna tukuandalie uje chakuja chaPasaka?" 18Wadakambila, "pitani kumjini kwa munthu fulani ni mkambileni, oyeluza wakamba, "nyengo yanga yakalibia siinimize Pasaka pamoji ni opuzila wanga mkati mwa pakomo pako." 19Opuzila adachita ngati Yesu umo wadakambila, ndi adaanda chakudya cha Pasaka.20Yapodafika ujula, wadankala kudya chakudya pamoji ndi opuzikakumi ndi awili. 21Yapo amadya chakudya wadakamba, "uzene ndi kukambilani kuti mmoji wanu siwani ukile." 22Adali ni chisoni sana ndi kila mmoji, wadayamba kumfancha, "Bwa, nde kuti osati ine, Ambuye?"23Wadajibu, "yuja ambayo wabizo jancha lake pamoji ndi ine mkati mwa bakuli nde vya siwani ukile. 24Mwana wa Mwanadamu siwachoke, ngati umoyalembedwa. Nampho ole wake munthu ambaye siwamuukile Mwana wa Mwanadamu! Idankala bwino kwa munthu mmeneyo siwadakabadwa." 25Yuda, mmeneyo uyo wadakamuukile wadakamba, "Bwa!, Ndi ine puzisi?" Yesu wadamkambila, "wakamba chinthu chimecho iwe umwene."26Yapo amadya chakudya, Yesu wadatenga mkate, wadaubaliki, ndi kuumeza wadaaninka opuzila wake wadakamba, "tengani mdye, ili ndi nthupi langa."27Wadatenga chikombe ni kuyamikila, wadaninkani kukamba, "mamwani wonche pakati pa ichi. 28Pakuti uunimwali wa lamula langa, itaidwa kwa ndande ya ambili kwa kulekeledwa ni vachimo. 29Nampho nikukambilani, sinimwacha matunda ya mzabibu uu, hadi sikulija sinimwe pamaji namwe kupitila ufumu wa Atate wanga."30Yapo adamaliza kuimba nyimbo, adachoka kupita kupili la mizeituni. 31Ndipo Yesu wadakambila, "usiku huu anyiimwe mwoncho simjikwale ndande yanga, pakuti yalembedwa, sinimbule awesa mbelele wa gulu satawanyike. 32Nampho Baada ya kuhyuka kwanga, sinikuchagaleleni kupita ku Galilaya."33Nampho Petro wadamkambila, "ata ngati wonche siakukane ndande ya vichita ivovikupate, ine sindikukana." 34Yesu wadajibu, "uzene nikukambila usiku uu kabla tambala siwadalile, siunikane mala katatu." 35Petro wadamkambila, "atangati ikankazekana kufa ndi iwe, sindikukana." ndi opuzila winacho wonche adakamba mchimwecho.36Pambuyo pake Yesu wadapita nao pamalo patanidwa Gethsemane ndi wadakambila opuzila wake, "nkalani yapa nyengo ninipita uka kupempha." 37Wadamtenga Petro ni wana awili a Zebedayo ndi kuyamba kundandaula ndi kuganizila. 38Ndipo wadakambila, "mtima wanga uli ndi chidandaula chachikulu sana, ata kiasi cha kufa, nkalani yapa mkeshe pamoji nane."39Wadapita pachogolo kidogo, wadagwa liali, ndi kupempha. Wadakamba, "Atate wanga, ngati ikalekana, chikombe ichi chiniepuke, isidankala ngatiumonifunila ine, nampho ngati umo mufunila imwe." 40Wadaendela opuzila ndi wadapela agona litulo ndi wadamkambila Petro, "ndande chiyanisimdakala kukesha nane kwa lisaa limoji? 41Koshani ndi kupempha dala msidalowa mmaesedwe mtima uli tayari, nampho ntupi ndo shida."42Wadapita lake mala ya kawili ndi kupempha, wadakamba, "Atate wanga, ngati chichito ichi sichikozekana kuniepuka ndi lazima nimwole chikombo ichi, malamula yako yachitike." 43Wadabwelancha wadaapela agano litulo, pakuti masa yao yadalemela. 44Ndeyapo wadasiyancho wadapita lake kupempha mara ya katatu niwakamba mau yayoncha.45Pambuyo pake Yesu wadaendela opuzila wake ndi kwakambila, "mkali mkugona tu ndi kupumulila? Penyani saa ikalibia, ni Mwana wa Mwanadamu siwaukilidwe mmamncha mwa ochimo. 46Ukani, tujichoka, penya, yuja waniukila wakalibia."47Nyengo adali akali mkukamba, Yuda mmoji wa anyiwaja kumi ndi awili, wadancha gulu lalikulu aliodancha pamoji naye nilichokela kwa wakulu anchembe ndi midala ya wanthu adaja ni maupanga ni vibanga. 48Tena munthu wadaganizila kumuukila Yesu wadaaninka ishala, wadakamba, "yuja sinikamule ndo mmwezo mgwileni."49Nyengo imeneyo wadaja kwa Yesu ndi kukamba, "nikulonjela, puzisi!" ndi kumbusu. 50Yesu wadamkambila, "Bwenohi, lichite lijambalo lakupeleka." Ndeyapo adaja ndi kumnyoshela jancha Yesu, ndi kumgwila.51Penya, munthu mmoji wadili pamoji ndi Yesu, wadanyosha jancha lake, wadachomaa upanga wake, ndi kumbulamtumika wa wamkulu wao nchembe, ndi kumdula nkutu lake. 52Ndeyapo Yesu wadamkambila, bwela upanga wako paja waunchoncha, pakuti wonche autumia upanga siangamizidwe ndi upanga. 53Mganizila kuti sindikoza kumtana tate wanga, nayencho kunitumila majeshi zaidi ya kumi ndi awili ya angelo? 54Nampho basi mtundu wanchi mau yadakakoza kutimizidwa, mchimwechi ndeuma ifunikila na kunichokela?55Nyengo imeneyo Yesu wadalikambila gulu, "Bwa! Mwaja ndi maupanga ndi vibanga kuigwila ngati mnkungu? Kila siku mimankala mkanisa niniyeluza, ni simdanigwile. 56Nampho yonche yaya yachitika ili mau ya olosa yatimizidwe." Ndeyapo opuzila wake adamsia ndi kutawa.57Anyiwancha adamgwila Yesu adampeleka ka Kayafa, wamkulu wa nchembe, pamalo ambapo olemba ndi midala yapoadapezana pamoji. 58Nampho Petro wamchata mmbuyo ka patali hadi pakati pa ukumbi wa wakulu anchembe. Wadalowa mkati ndi kunkala pamoji ndi alinda waone ichasichichokele.59Ndeyapo waklu anchembe ndi bwalo lonche adafunafuna ushahidi w mtila pakati pa Yesu, dala kuti apate kumwimpha. 60Licha kuti adachokela mashahidi ambili, nampho siadapate ndande yaliyonche. Nampho pambuyo pake mashahidi awili adajitokeza panchogolo. 61Ndi kukamba, "munthu uyu wadakamba, nikoza kutyola kanisa la Mlungu ndi kumangancha kwa siku zitatu."62Wamkulu wa nchembe wadaima ndi kumfuncha, "siukoza kujibu? Anyiyawa akushudia chiyani pakati pako?" 63Nampho Yesu wadankala kachete, wamkulu wanchembe wadamkambila, "ngati Mulungu umowashila ndikulamula utukambile ngati iwe ndi Kristo, Mwana wa Mulungu." 64Yesu wadajibu, "iwe wamwene wakamba chinthu chimonecha. Nampho nikukambila, kuchokela saino ni kuendelea siumuone Mwana wa Mwanadamu wankala nchancha la kuchimuna la mphavu ndi waja kupitila mitamba ya umwamba."65Ndeyapo wamkulu wa nchembe wang'amba nchalu zake ndi kukamba, "watukana! Bwa, tufunancho ushahidi wa chiyani? Penya, tayari mwavela ndi watukana. 66Bwa! Mganizila chiyani? adajibu ndi kkamba, "wastahili kupedwa?"67Ndeyapo adamlavulil malovu pamaso ndi kumbula nkonyo, ndi kumchapa makofi kwa mancha yao. 68Ndi kukamba, "tulasele, iwe Kristo ndi yani wakunchapa?"69Nyengo imeneyo Petro wadankala kubwalo kwa bwalo, ndi mtumiki wamkazi adamchota ndi kukamba, "iwe nawe udali pamoji ndi Yesu wa Galilaya." 70Nampho wadakana pachogolo pao wonche, wadakamba, sindijiwa chinthu icho ukamba."71Nyapo wadapita kubwalo la kamo, mtumiki mwina wamkazi wadamwenandi, kwaakambila udilipamenepo, "munthu uyu naye wadali pamoji ndi Yesu wa Nazareti." 72Wadakana acha kwa kulapa, "ine sindimjiwa munthu uyu." "73Nengo yayifupi pambuyo pake, anyiwancha adaimajilani, adamnchata ndi kukamba ndi Petro,"kwauzene iwe nawe uli mmoji wo, pakuti atakambidwe laka likulangiza." 74Ndeyapo wadayamba kukamba ndikulapa, "ine sindimjiw munthu uyu, " ndiyenga imweyo tambala wadalila. 75Petro wadakumbuka mau wadakambilidwa ndi Yesu, kabla tambala siwadalile siunikane mara katatu."

Chapter 27

1Umawa yapo kudacha wakulaakulu anchembe wonche ndi midala adapangana kuti amuphe Yesu. 2Adammanga, ndikumchogoza ndikumfikiza kwa Pilato.3Yuda yapowampeleka Yesu kwa aani, wadaona kuti watolangidwa, wadadandaula ndi kubweza ndalama makumi yatatu kwa wamkulu wa nchembe ndi mdala. 4Ndikukamba, ndalakwa kugulicha mwaziuoulijhe ndande, nampho adayankha ife tilijhe nazo kanthu izo ndi zako! Uone umwene. 5Wadazimwaza panchi ndalama makumi yatatu mkati mwa nyumba ya mapemphelo, ndikuchoka kupita kujipha.6Mkulu wanchembe wadatenga zijha ndalama makumi ya tatu ndi kukamba, osati zene kuziika ndalama izi mbokosi la chuma chifukwa chake ndi nthengo wa magazi. 7Adawana kuti ndalama agule munda wakuazikhila alendo. 8Pachifukwa ichi munda umeneo utanidwa munda wa magazi mbakana lelo.9Lijha mau wadakamba mlosi Yeremia lidakwanila, kunena, "adatenga ndalama makumi ya tatu, nthengo udapangidwa ndi wanthu aku Israel ndanda ya iye. 10Ndikutumikila kunda, ngati ambuye umo adalamulila."11Adamuimikila Yesu pachogolo pa Pilato, ndi Pilato wadamfuncha, Bwanji. Iwe ndefumu ya Ayahudi? Yesu adayankha iwe nde ukamba chimwecho. 12Nampho yap wamaimbidwa mlandu ndi wakuluakulu anchembe ndi midala Yesu sewadayankhe mau. 13Pilato wadamkamba, siuvela milandu uimbidwa? 14Nampho siwadayankhe mau lalilonche,kwa icho Pilato wadali odabwa kupunda.15Pa nthawi ya chikondwelero mtethe wa Pilato udali kummasula omangidwa mmojhi uyo wasankhidwa ndi gulu. 16Nyengo imeneyo wadalipo omangidwa mwina wamajhiwika ngati Baraba.17Yapo adakomana pamojhi, Pilato wadafuncha yani mfuna ndikumasulileni? Baraba kapina Yesu watanidwa Kristo? 18Ndande wadajhiwa kuti athokumghwila ndande ya kuda kwa mitima yao. 19Yapo wamakhala pampando wake wa malamulo. Mkazake wadamtumizila maundi kukamba usamchita choipa chalichonche munthu mmeneyo wolungama. Chifukwa chake ndavutika kupunda kulitulo chifukwa cha munthu mmeneyo.20Ndeyapo wakuluakulu anchembe ndi midala adayamba kwa akakamiza wanthu kuti amphemphe Baraba ndi Yesu waphedwe. 21Pilato wadafuncha, kuti pa awili yawamfuna ndikumasulileni? Adakamba Baraba. 22Pilato waadafuncha ndimchitenji Yesu watanidwa Kristo? Wonche adayankha wawambidwe pamtanda.23Iye wadafuncha ndande chiyani, walakwa chiyani? Nampho adakweza mau kupunda kti wawambidwe. 24Pilato yapowadaona siwakhoza kuchita chilichonche, pambuyo pake padayamba chipwilikiti wadatenga majhi wadasamba mmajha pa maso pagulu ndi kukamba ine sindiona kula kwa munthu uyu, onani izi mwachinawene wake.25Wanthu wonche adakamba mwazi wake ukhale ndiife ndi achanawatu. 26Pambuyo pake wadammasula Baraba, ndi Yesu kummenya vikoti, adapachidwa Yesu ndikupita kumuwamba pa mtanda.27Asilikari a Pilato adamtenga Yesu mbakana ku Praitorio ndi gulu lalikulu la Asilikari adakhomana pamojhi. 28Adamvula nchalu zake ndikumveka chivalo chofuwila. 29Adakonja chisoti cha minga ndikumveka, adamwikila nchungwi janjha lake la kwene.30Adamlavulila malovu ndi kutenga nchungwi kummenya nayo kumuthu. 31Yapo amamchita chipongwe, adamvula chivalo ndikumveka vivalo vake ndikuchogoza kupita kumuwamba.32Yapo adatuluka kubwalo adamuona munthu wa ku Krene watanidwa Simeoni iye adamkhkaniza kuchogozana nao kuti wakhoze kunyamula mtanda. 33Yapo adafika pamalo patanidwa Goligotha, mate yake chibade cha mutu. 34Adamphacha vinyo yasingizikana ndi ndulu kuti wamwe nampho yapho wadalawa siwadakhoze kumwa.35Yapo wadawambidwa pamtanda, adagawana vivalo vake ndikuvichitilachisankho. 36Ndi adakhala kumphenyelela. 37Pamwamba pa mutu wake adaikapo milandu iyo imawelengeka, uyu nde Yesu fumu ya Ayahudi."38Achifamba awili adawambidwa pamojhi ndi iye, mmojhi jhanja la kwene ndi mmojhi janjha la manjele. 39Anyiao amapita njila adamnyodola, ndi kutingiza mitu yao. 40Iwe umafuna "kugomola nyumba ya maphemphelo ndikumanga mwa masiku ya tatu, jiombole umwene ndi ngati mwana wa Mulungu chikha pa mtandapo.41Wakuluakulu anchembe adamseka , pamojhi olembela pamojhi ndi midala, ndi kunena. 42Wadaombola wina,nampho walepela kujhiombola mwene wake. Iye ndifumu ya Ayahudi basi wachikhe pamtandapo ife timkulupalile.43Wadakulupalila Mulungu, siyani wamuombole chiphano ngati wafuna, ndande wadakamba, ine ndi mwana wa Mulungu. 44Achifwamba wajha adawambidwa pamojhi ndi iye nao amakamba mau yakumseka.45Kuchokela pa nyengo 12:00 kudali mdima mbakana 3:00. 46Pa nyengo ya 3:00 Yesu wadalila kwa mphamvu Eloi, Eloi lamasabakhtani! Kuti Mulungu wanga Mulungu wanga wandisia nji? 47Akamojhi adaimaima pajha adavela, amakamba wamtana Eliya.48Mmojhi wadatamanga ukatenga chinkhupule ndikutilamo chakumwa chowa ndi kuika pachogolo pa mtengo ndi kumkwezela kuti wamwe. 49Wina adakhalila amakamba, msiyeniyokha tione ngati Eliya siwajhe kumuombola. 50Yesu wadalilancho kwa mphamvu ndi kumwalila.51Onani, chinchalu chochinga nyumba ya Mulungu chidangambika vibanthu viwili kuchokela kumwamba mbakana panchi, dothi lida thenthmela miyala idasweka vibanthu vibanthu. 52Viliza vida vunukukha, mathupi ya wanthu oyera ambili yao adagona litulo adanchidwa. 53Adachokela kuviliza pambuyo pohyuka kwa iye adalowa mmujhi oyera, ndi adaoneka ambili.54Yujha wamkulu ndi anyiwajha amamphenya Yesu adaona chimtingiza, ndi vinthu ivo vidachokela adali ndi mantha kupunda ndikunena, zene uyu wadali mwana wa Mlungu. 55Wachikazi ambili adamchata Yesu kuchokela ku Galilaya kumtumikila adali pajha kuchokela patali. 56Mkati mwao wadalipo Mariamu Magdalema, Mariam amake a Yakobo ndi Yusufu, ndi mai wawana a Zebedayo.57Ujhulo wadajha munthu olemela kuchokela ku Arimathaya, uyo wanatanidwa Yusufu, naye wadali omphuzila wa Yesu. 58Wadampitila Pilato ndi kumphempha thupi la Yesu, Pilato wadalamula waphachidwe.59Yusufu wadatenga thupi ndikulimanga ndinchal yoyera. 60Ndikuligoneka mchiliza cha chiphano icho wadajhikonjela pa mwala, ndikulivinikila ndi mwala waukulu pa komo la chiliza ndi kuchokapo. 61Mariamu Magdalena ndi Mariamu yujha mwina adalipajha, maso yao amapenya kuchiliza.62Siku lidachatila, idali siku pambuyo pokonyekela, wakuluakulu anchembe ndi Afarisayo adali pamojhi kwa Pilato. 63Adamkambila, "Ambuye, tikumbukila kuti yujha waunami wali wamoyo, wadakamba pambuyo pa masiku ya tatu siwahyuke." 64Kwaicho lamula kuti chiliza chipenyeleledwe bwino mbakana siku la katatu ngati sichimwecho omphuzilra wake sakambe ndikunena kwa wanthu wauka kuchokela kwa akufa, ndinami othela kukhala oipa kuposa oyamba.65Pilato wadaakambila tengani openyelela mapitani mkapenyelele bwino bwino umosinkhakozele. 66Kwaicho adapita kukapenyelela chiliza mwala udaikidwa chidindo ndikuika openyelela.

Chapter 28

1Pambuyo ufulu siku la sabato, juwa yapo lidali ndilibila kupita kusikulo yamba ya juma, Mariamu Magdalena, ndi yuja Mariamu mwina adaja kuchipenya chiliza. 2Penya kudali ndi tendemelo lalikulu, pandande angelo wa Mulungu adachika ndi kuvilinga uja mwala, ndipo wadalikalila.3Ngope yake idali ngati yamangesi, ndi vovala vake yodali yoela ngati theluji. 4Waja opuzila adajala manda ndikukala ngati afa.5Yuja angelo wadakambila waja wachikazi ndikukamba, "msidaopa pakuti ndijiwa kuti mumchota Yesu, uyowadapedwa. 6Palibepo pano, nambo wauka ngati umowa dakukambilani bwelani muone pamalo yapo ambuye adagona. 7Pitani chisanga mkakambile opuzila wake, "awauka kuchoka kwa akufa, penyani wakuchogolelani Kugalilaya. Kumene ndiko simumuone penani ine nakukambilani."8Waja wachikazi adachoka paja pachiliza chisanga alindimanda ndi chisangalalo chachikulu, ndi adatamanga kwakambila opuzila wake. 9Penya Yesu wadapezana nao ndikukamba, "salamu." Waja opuzila adabwela ndiuja kugwila myendo yake ndipuso kumwabudu. 10Ndipo Yesu wadakambila, "msidaopa, pitani mkakambile abale wanga achongole Kugalilaya. Kumene sanione.11Ndawi imene wachikazi amapita, penya ochepa wa olinda adapita kumjini ndi kwakambila wakulu amakuhani vindu vonje vidali vachitika. 12Nao makuhani yapoadali apezana ndi azee ndikulikambilila chindu icho pamoji nao, nao adachocha kiasi chachikulu cha ndalama kwawaja askari. 13Ndi kwakambila, "aambileni wina kuti, opuzila a Yesu adabwela usiku ndikuuba tupi la Yesu ndawi ife tangona."14Ngati khani iyi siifikile wakulu, ifesitimmnamize ndi kukuchokelani anyiimwe kuopa koje. 15Ndipo waja askali aditenga zija ndalama ndikuchita ngati ivo akambila khani iyi idapita sana kwa Ayahudi ndi yakala chocho mbaka lelo.16Nambo waja atumiki kumi ndimmoji adapita Kugalilaya, kuja lija pili kuja wadakambila. 17Nao yapo adamuona, adamwabudu, nambo ochepa wao awakaika.18Yesu wadabwela kwao ndikwa akambila ndi kukamba, "maningidwa malamulo yonje pajiko ndi kumwamba. 19Kwaicho maptani mkaachite wantu ajikolonche kuti oyaluzidwa abatizeni mwajina Baba ndi la Mwana ndila Mzimu Oyela.20Ayaluzine kuzigwira nkani zonche ndakulamulani ndipenyani ine ndili pamoji namwe ntawi zonche ingakale kumaelo kwa jiko."

Mark

Chapter 1

1Ichi ni chiyambi cha utengu wa Yesu Mwana wa Mulungu. 2Ngati umeyalembedwela ndi orota Isaya, "peuya ndi mtumalutenge wange pachogolo pako mmoji wokonja njira yako. 3Mau ya mvufu walipandenga denga ikonjezelewi njira ya fumu zitaudalikewi njila zake."4Yohana wadaja ndi wabatize mtengo ndi kukambilila ubatizo wolapa ndi kulekeledwa machinwo. 5Siko lonche la Yudea ndi wantu wonche wa Yerusalemu atapita kwanye adeli ndi abatizwa ndiiye pakati pamchinje Yordani ndi achila machimo yao. 6Yohana wadele ndi chovala che mabweya ya ngamia ndi lamba la chikwetu mchiuno mwake ndi wa dali ndi wadya jombe ndi uchi wa mtengo.7wade kaubolila ndi kukauba ''walipo mawofi wakuja'' pambuyo paine wali ndi mphavu zambili lapunde zaiwe ndi ndilije ulemelelo wa kukwatama pauche ndi kumanga malemba ya vilato vake. 8Ine nidakubatizawi kwa majo nampo iye siwa kubatizwe kwa Mzimu Oyela."9Idachokele nyengo zimenezo kuti Yesu wadaja kuchokela Kunazaleti ya Galilaya ndi wadebatizidwa ndiyo hawa pa mchiye wa Yordani. 10Ntawi Yesu waukakuchokela mmaji wadeona jiko la fimpana masomaso ndi Mzimu ndi uchike Panchi pamwamba pake ngati nkunda. 11Ndi mau yadachoka kumwamba, "iwe nde mwana wanga okondedwa nawe kupunda."12Pambuyo pake ntawi kamoji mtima ude mwinikisa kupita mtengo. 13Wadali mtengo masiku arobaini ndiwa yesedwa ni satana wadali ndi zinyama za mtengo ndi angelo ademtandiza.14Chapamo pambuyo payohama kungwidwa Yesu wadaja Kugalilaya ndi wayakamba mau ya Mulungu. 15Wawakamba, "ntawi ya kwana ndi Ufuru wa Mulungu wawandikila lapani ndi kuwemeleza pakati pa mau ya Mulungu.''16Ndi ndiwaenda mpepete mwa nyanja ya Galilaya wada muona Simoni ndi Andrea mbale wake Simoni ndi ataya makokavyao mkati mwa nyanja pakati adeli ovua. 17Yesu wadaakambila "majani wichateni," ndi sindikuchiteni ovua wantu. '' 18Ndi ntawi kameji adefia makoka ndi kumchata.19Ntawi Yesu yapo wadeyeude utali pangone wade muone Yakobo mwana wa Zebedayo ndi Yohana mbale wake adali mbwato ndi atumiki ndi akonja makoka. 20Ntawi wade atana naoncho adewisia tata wao Zebedayo mkati mwa bwato ndi atumila adepangilidwa ada mchata.21Ndeyapo adafika kaperinaumo siku ya sabato Yesu wadolowa mopempelela ndi kuyaluza. 22Adazizwa mayaluzo yake chifuko wampayaloza ngati muntu wali ndi malemulo osauti ngati olemba.23Ntawi yomweyo kudeli muntu mkati mwa nyumba ya mapempelo wadeli ndi mtima wakude ndi wadeyamba mapokoso. 24Ndi wakamba "tilindichiyani choelita ndiiwe Yesu wa Nazareti? waja kuti pweteka? ndikujiwa uliyani iwe ndi oyela wa Mulungu wake. 25Yesu wada mkanisa wa mtima wakude ndi kukamba kachete ndi uchoke mkati mwake. 26Mtima wakude wadengwecha panchi ndi wadechoka kwaiye ndwalila kwa mau yakwezeka ya pamwamba.27Ndi wantu wonche adezizwa mmwemo ada fuchana mmoji ndi mnjake, "ichi ndi chiyani?" Yaruzo la chapamo lili ndi lamulo? Ata wazilamule pempo zoipa ndizi mvemele. 28Ndinkani zaiye ntawi yochepa zede yende tumalukatikoa wa Galilaya.29Ndi ntawi kamoji pambuyo pochoka mkati mwa nyumba ya mapempelo adalowa mnyumba ya Simoni ndi Andrea ali ndi Yakobo ndi Yohana. 30Chapawa apongoziwakewa Simoni wadali wagona odwela matende ndi utawi pang'ono ada nkambile Yesu nkhani zake. 31Mmwemo wadaja ndeku mguli ndi maja ndikuakweza mmwamba matende ya dechoka kuiye ndi wadayamba kwa taudize.32Ujulo umweo ntawi fua lato kubila ada mpelekela kwaiye wonche adali odwala kapewe adali ndi pempo zoipa. 33Mujowonche adakalila limoji pa chicheko. 34Wade alamicha ambili adali odwala matendo ya mtundu, mtundu ndi kuchocha mpepo zoipa za mbili ikapauda siwada vemeleze mpepo zoipa kukamba chifuko zimamjiwa.35Wadaoke umava mava kukali ndi mdimo wada choka ndi kupita kumalo kwa yenka ndi wamapempelo kumeneko. 36Simon ndioche adal pamoji naye adamchata. 37Adampeza ndikumkambila, "waliyenche wakufunafuna."38Wada akambila tuyeni malo yena kubwalo kwa muji zungulila dala kuti ndikoze kupeleka mai kumeneko nako ndiye chifukwa ndidajha pahoncho. 39Wadapita ndi kupitila mu Galilaya yonche ndi wkama pakati pa malo ya mapempelo ndi wakaniza mpepo zoipa.40Wamakate mmoji wadaja kwaiye wadali ndi wa mpempa wagwada ndi wadamkambila, "ngati ufumu na ukoza kundi chita ndi kale bwino." 41Ndi wakangizidwa ndi lisungu Yesu wadatandalika janjalake ndwakutomasa ndiwa mkahila ndifuna ujalebwino. 42Ntawi kumeji makate yadechoka ndiwa dachifidwa wakale wa bwino.43Yesu wade mkasa kupande wade mkuwahi mapita ndei inwesho. 44Wade mkaubila "jipenyelele usadokumbamau kwa waliyeuche nampo mapota ukaji lauguze kwa padre ndioke choche yamiko la kuchitindwa wabwino limene Musa wada kumbi lila ngati langizo kwa anyiiwe .''45Nampo watapita ndikuyamba kwaaka mbia waaliyenche ndi kumwaza maukupunda mpaka Yesu suwada kozekuluwa mojo kwa ufuru mmwemo wadakala pampepete payekayeka ndi wantu adaja kwaiye kuchokela mmalo mwa mfuadu mtuudu.

Chapter 2

1Yapoadabwela Kukapernaumu pamvbuyo pa masihi yochepa, idveka kuti wadali kukomo. 2Wandhu ambili kupunda adi asoghana pajha ndi sipanalepo malojho, ataijha ya pajha pakomo, ndi Yesu adakamba mau kwanyiiwo.3Ndipo akumoji a wandhu adajha kwaiye adampeleka mundhu wadali apoloza. Wandhu anayi adafi kumbala. 4Nyengo adalepela kumwandikila chifuko cha gulu la wandhu adachocha chindu kumwamba pamalo pajha adalipo. Ndi yapo adatomaliza kutoola malo, adachicha chitanda icho mundhu opoloza wadali wagona.5Yapo wadapenya chikulupi chao, Yesu adamkambila mundhu apoloza, "mwanawanga, machimo yako yalekeleledwa." 6Nampho akumojhi ya wandhu adali akala pajha adamfujhafujha mmitima mwao. 7''Wakoza bwanji mundhu uyu kukama chimwechi? Wapepula! Yani wakoza kumlekelela machimo ikapanda Mulungu yokape?''8Pamwepo Yesu wajajhiwa mutima mwake icho aganizila mwa mmojhi mwa achinawene. Adakambila, "kwa chiyani mganizila chimwechi mmitima mwanu?" 9Liti lopepuka kupunda kunena kwa mundhu uyo wapoloza machimo yako yalekeleledwa, kapena kunena, "imatenga chitenda chako, ndi uende?'10Nampho kuti apeze kujhiwa ya kuti mwana wa Adamu wali ndi malamulo ya kulekelela machimo mujhiko, adamkaambila yujha wadapoloza. 11Ndikukambila iwe, nyanyuka, tenda mkeka wako, ujiwela kukomo lako. 12Adayima ndi mara kamojhi adatenga mkeka wake,ndi kupita kubwalo kwa nyumba pa chogolo pa kila mundhu mmwemo, wonche adadabwa ndi kumpacha Mulungu ulemelelo, ndi kunena, "ndivitu sidaonepo kuona chindhu ngati ichi."13Wadapitancho mmphepetete mwa nyanja, ndi gulu lonche la wandhu adajha kwaiye, ndi kuwayaluza. 14Yapo wamapita adamwona Lawi mwana wa Alfayo wakala pamalo pa kulandilila sogho ndi kumkambila, "nichate." Wadaima ndi kumchata.15Ndi nyengo Yesu yapo wamadya chakudya mnymba ya Lawi, olandila sogho ambili ndi wandhu adali ndi machimo adalindi adya ndi Yesu ndi opunzila wake, pakuti adali ambili nawo adamchata. 16Nyengo olemba, yawo adali Mafarisayo, yapoadaona kuti Yesu wadali kudya ndi wandhu amachimo ndi osoga sogho, adakambila opunzila wake, "ndande chiyani wakudya ndi osagha sogho ndi wandhu yawo amachimo?"17Nengo Yesu yapowadavela chimwechi adakambila, "wandhu yawo ali ndi tanzi mtuphisiafuna chitetezo, ndi wandhu odwala okandiwo afuna. Sindidajhe kwatana wandhu yawo achilongamo, nampho wandhu ali ndi machimo."18Opunzila wa Yohana ndi Mafarisayo adali kumanga ndi akumojhi wa wandhu adajha kwaiye ndi kumkambila, "ndande chiyani opunzila Yohana ndi Mafarisayo kumanga. Nampho opunzila anyiwe umanga. 19Yesu adakambila, "Bwanji yawoadawndikila paukwati akoza kumanga nyengo wa mkulu wa ukwati yapo wakala wakati wadi pamojhi ndi anyiiwo siwakoza kumanga."20Namphomasiku siyajhe nyengo wamkulu wa ukwati yaposiwachochedwe anyiiwo, ndipo siku zimenezo anyiiwo siamange. 21Palibe mundhu wasoka hipande cha mpya cha njalu pa chovala cha kutaita, panapo chigamba siching'anamuka kuchoka pamenepo, champya kung'ang'anamuka kuchoka pa chakutaita ndi sipakalepo mngiasi oyipa.22Palibe mundhu watila mvinyo chipano mu chikombe chaa kale, pana pake mvinyo sing'ambe vikombe ndi vonche viwili mvinyo ndi vikombe sivitaike. Penapo ika mvinyo wa chipano muvikombe vachipano."23Pa siku ya sabato Yesu wadapita mmojhi mwa minda ndi opunzila wake adayamba kutenga ya mojhi ya vipute vangano. 24Ndi Mafarisayo adamkambila, "penya, ndande chiyani achita chinthu icho chili kumbuyo kwa matauko ya masiku ya sabato?"25Adamkambila, "simdasome chijha wadachicha Daudi yapowadali pakufuna ndi njala - iye pamojhi ndi wandhu yao adali pamojhi ndi iye? 26Umo wadapitila munyumba ya Mulungu nyengo Abiathari yapowadali wamkulu wa nchembe ndipo wadadya mikate iyoidaikidwa pachogolo iyo idali osati malinga ya matauko ya mundhu waliyenche kudya ikakala wanchembe ndi kuwapacha akuojhi ya anyiwajha adali pamojhi ndiiye?"27Yesu wadanena, "sabato idachitidwa kwa ndande ya achiwandhu, osati wandhu kwa ndande ya sabato. 28Kwa icho mwana wa Adamundi wamkulu mpakana kwa Sabato."

Chapter 3

1Ndi wadalowa mkati mwa Sinagogi kudali ndi munthu opoloza janja. 2Akumoji amamchatilila kwa pafupi kuona ngati siwamchilise siku la sabata kuti amuimbimbe mlandu.3Yesu wadamkambila munthu opolozayu ima pakati pa guruli. 4Ndipo wadakambila wanthu, "bwa zoona kuchta vichito va bwino siku la Sabata kapena kuchita vopande malinga, kupulumucha umoyo kapena kupa?" Nampho adakala kachete.5Wadaapenya kokwiya ndi kwa chisoni ndande ya kulimba kwa mitima yao, ndi kumkambila munthu yuja tambasula janja lako, wadatambasula ndi Yesu wadamlamicha janja lake. 6Mafarisayo adapita kubwalo ndi kupanga ndi Maherode kuti amphe.7Ndipo Yesu ndi opunzila wake, adapita kunyanja ndi gulu la wanthu lidaachata lochokela Kugalilaya ndi Kuyuda. 8Ndi kuchoka Kuyerusalemu ndi kuchoka kuidumaya ndi kuchogolo ya Yordani ndi pafupi pa Tiro ndi Sidoni, gulu lalikulu yapo lidavela vonche ivo wavichitalidaja kwa iye.9Nde wadaakambila opunzila wake kuti ampenyele bwatowaung'ono ndande ya gulu kuti angampinye. 10Chifuko wadalamicha ambili, kila munthu wali ndi mavuto wadafuna wamfikile ndi kumkavya.11Paliponche mizimu ya ukadili ikamuona, idagwa panchi pachogolo pake ndi kulil ndi kukamba, "ie ndi Mwana wa Mulungu." 12Wadaalamula ndi kuachimikiza asadachita wajiwike.13Wadapita pamwamba pa pili ndi kuatana yao wadaafuna ndi adapita kwaiye. 14Wadaasankha kumi ndi awili (wadaatana otumidwa) kuti akale pamoji ndi iye ndi wakoze kuatuma kulalika. 15Ndi lamulo lolocha mizimu yoipa. 16Ndi kuasankha kumi ndi awili, Simoni wadampacha jina la Petro.17Yakobo mwana wa Zebedayo ndi Yohana mbale wake, wadaapacha jina la Bonagesi, mateyake wana oluluma, 18ndi Andrea, Filipo, Bartholomayo, Mathayo, Tomaso, Yakobo mwana wa Alfayo, Thadayo, Simoni Mkananayo, 19ndi Yuda Iskariote uyo siwamuukile.20Ndipo wadapita kunyumba kwake ndi gulu la wanthu lidaja pamojincho, mbaka adalepela kudya mkate. 21Ambali yake yapo adapata nkhani adapata nkhani adapita kumgwila pakuti adanena walindi msala. 22Olemba adaja uchoka Kuyerusalemu adakamba, wali ndi Beelzebuli ndi wachocha mizimu yoipa kwa lamulo la wamkulu wa mizimu yoipa.23Yesu wadaatana ndi kukambanao mwa chifanizo, Satana wakoza kumtopola Satana? 24Ngati ufumu wadakana wene ufumu umeneo siukoza kuima. 25Ngati ufumu wdakana wene ufumu umeneo siukoza kuima.26Ngati satana siwaima bwino muufumu wake siwakoza kuima ndi ufumu wake siufikile potela pake. 27Nampho palije hata mmojhi wakoza kulowa mnyumba ya munthu wali ndi mphavu ndi kuba vinthu vake popande kummanga wali ndi mphavu huti ndi kukusa vili mnyumbamo.28Zene nikukambilani machimo yonche ya wana awanthu siyakuhulukidwa, 29nampho walienche wamkambila mau ya ukadili Mzimu Oyera siwakululukidwa, nampho siwakale ndi chimo la muyaya. 30Yesu wadakamba mauti ndande amakamba, "wali ndi Mzimu oipa."31Ndipo amai wake ndi abale wake adaja ndi kuima kubwalo, adamtuma munthu kumtana. 32Ndi gulu la wanthu lidakala pafupi naye adamkambila, "amai wako ndi abale wako ali kubwalo, akufunafuna iwe."33Wadaayankha, "amai wanga ndi abale wanga ndi achiyani?" 34Wadaapenya yao adakala ndi kumzungulila, ndi kukamba penyani anyiyawa nde amai wanga ni abale wanga. 35Walienche wachita chikondi cha Mulungu, munthu mmene nde m'bale wanga, mlongo wanga ndi mai wanga.''

Chapter 4

1Ndipo wadayamba kuyaluza mmphepete mwa nyanja. Ndi gulu lalikuli lidasonkhana lidmzungulila, wadalowa mkati mwa bwato mnyanja, ndi kukhala, gulu lonche lidali mmphepete mwa nyanja mmasekwa. 2Ndi wadayaluza vinthu va mbili kwa chifanizi ndi wadakamba kwa anyaio kwa mayaluzo yake.3Vechelani ovyala wa dapita kuvyala. 4Yapowadali niwavyala mbeu zina zidagwa mnjila ndi mbalame zidajha zidadya. 5Mbeu zinjake zidagwela pa mwala yapopadalibe dothi la mbili mala zidafyota kwa chifuko zidalibe dothi lokwana.6Nampho jhua yapo lidatuluka, zidafyota ndi kwa chifuko zidalibe mizo, zidauma. 7Mbeu zinjake zidagwela pakatikati pa minga. Minga zidakula ndi zidazidoola, ndi sizidabale vipacho valivonche.8Mbeu zinjake zidagwa padothi la bwino ndi zidabala vipacho nyengo zimakula ndi kuongezeka, zinjake. Zidabala mala thelathini kupunda, zina zina sitini ndi zina mia. 9Ndi wadakamba, "waliyonche wali ndi masikio yakuvechela, ndi wavechele!"10Yesu yapo wadali yokha, anyiwajha adali pafupi nae ndi anyiwajha kumi ndi awili adamfuncha kukhuza vifanizi. 11Wadakamba kwa anyaio, "kwanu mwapachidwa chisisi cha ufumu wa Mulungu. Nampho kwa anyiyao ali kubwalo kila chinthu ndi chifanizi, 12kuti akapenya nde umo apenya, nampho saona ndi kwachimwecho yapo adavela nde umo avela, nampho savana navo, ngati osati adakang'anamuka ndi Mulungu adakaalekelela."13"Ndi wadakamba kwa anyaio, bwa simudavanenavo, chifanizi ichi? simukhoze kuvana navo vifanizi vinjake?" 14Ovyala wadavyala mau. 15Wina nde wajha adagwa mmphepete mwa njila pamalo mau yapolidavyalida ndi yapo adavela mala satana wadajha ndi kulitenga mau ilo lidavyalidwa mkati mwao.16Ndi wina ndi anyiwajha adavyalidwa pamwamba pa mwala, anyiyao, yapo alivela mau, kwa chisanga alilandila kwa chisangalalo. 17Nda alibe mizo yaliyonche mkati mwao, namho alimbikila kwa nyengo ya ifupi. Nampho mavuto ndi uchauchi yapovikujha kwa chifuko cha mau, mala kujhikuwala.18Ndi wina ni anyiwajha adavyalidwa pakati pa minga, alivela mau. 19Nampho usauchi wa jhiko, kunyengedwa kwa chuma, ndi kumbilo la vinthu vina, lalowa ndi kuliphika mau, ndi lilepela kubala vipacho. 20Ndipo kuli anyiwajha anyiyao adavyalidwa padothi la bwino. Alivela mau ndi kulilandila ndi kubala vipacho:wena wake thelathini, wena wake sitini, ndi wena wake mia mojha.''21Yesu wadaakambila, "bwa mupeleka nyali mkati mwa nyumba ndi kuiika panchi pa mseche, kapena panchi pa chithanda? Ipelekedwa mkati ndi kuiika pamwamba pa kiango. 22Pakuti palibe chalichonche icho chajhibia sichijhiwikana, ndi palibe chisisi icho sichiikidwa pa danga. 23Wakahalapo mwene masikio yakuvelela, ndi wavele!"24Wadaakambila, "khalani amphawi kwa chijha muchivela, pakuti chipimo ichompimila, nde icho simpimidwile ndi siongezedwele kwanu. 25Kwa ndande iye walinacho, siwalandile kupunda ndi yujha walibe, kuchokela kwake sivitengedwe ata ivo walinavo."26Ndi wadakamba, "ufumu wa Mulungu wafanizidwa ndi munthu wadavyala mbeu pakati pa dothi. 27Yapo wadagona usiku ndi kuuka umawa, ndi mbeu zidamela ndi kukula, ingakale siwajhiwa umo idachokela. 28Jhiko lichocha mbeu lene; poyamba machamba, alafu maduwa, alafu mbeu izo zakwima. 29Ndi nyengo mbeu yapo sikule yapya, mala kupeleka chisenga, kwa chifuko mavuno yakwanila."30Ndi wadakamba, "tiufanize ufumu wa Mulungu ndi chinthu chanji? Kapen titumikile chifanizi chanji kuukambilila? 31Ni ngati mbeu ya haradali, yapo idavyalidwa ni yaing'ono kupunda kupitilla mbeu zinche pajhiko. 32Ata, nyengo yavyalidwa, ikula ndi kukhala yaikulu kupitilila mimela yonche ya m'bustani, ndi ichita nthawi zazikulu, ata mbalame za kumwamba zikhoza kukonja visa vao mumtunchi wake."33Kwa vifanizi vambili wadayaluza,ndi wadakamba mau kwao, kwa umo adakhozela kuvechecha. 34Ndi kukamba nao popande chifanizi, nampho nyengo wadali yokha, wadaakambilila kila chinthu opuzila wake.35Pakati pasiku limenelo, nyengo ya ujhulo yapo udafika, wadakamba kwa anyaio, "tieni chijha la kawili." 36Chimwecho wadalisia gulu, adamtnga Yesu, nyengo imeneyo tayali wadal mkati mwa bwato, mabwato yanjake yadali pamojhi nae. 37Ni mphepo yo ng'ang'ala ya mwela ndi mafunde yamalowa mkati mwa bato ndi bwato tayali udali wajhala.38Nampho Yesu mwene wadali kwene shetri, wagona paphilo, adamuucha, adakamba, "abusa" simutengela mathe ife tikufa? 39Ndi wadauka, waaikalipila mphepo ndi wadaikambila nyanja, "ikale shwali, ntendele." Mphepo idalapa, ndi kudali kupola kwa kukulu.40Ndi wadakamba kwa anyaio, ndande yanji muopa? Bwa mulije chikhulupi mukali? 41Adajhalidwa ndi mantha yayakulu mkati mwao ndi adakambana anaio kwa anyaio, "uyu ni yanincho? Kwa chifuko ata mphepo ndi nyanja va mvela?"

Chapter 5

1Adaja mpaja upande wina wa nyanja, katika jiko la Gerasi. 2Ndi ghaFla nyengo Yesu yapowadali wamachokankubwalo kwa bwato, munthu mwene mtima oipha wadaja kwake kuchokela kumakaburi.3Muntu uyu wadalama pakaburi. Palibe uyo wadakoza kumchekeleza kupunda, palibe ata kwa vingwe. 4Wadali wamangidwa nyengo yambili kwa pingu ndi minyororo. Wadaidula minyololo ndi pingu zake zidaswedwa. Palibe hata mmoji uyowadali ndi mphavu za kumkoza.5Usiku ndi usana wadali kumakaburi ndi kumapili wadalila ndi kujidula iye mwene kwa myala ya kutwa. 6Yapowadamuona Yesu kwa kutali, wadamtamangira kwake ndikukwatama pachogolo pake.7Wadalila kwa sauti yaikulu, "uuna nikuchitile chiyani, Yesu mwana wa Mulungu wali kumwamba sana? Ndikutondoza kwa Mulungu mwene, siudamtesa." 8Pakuti wadali wamkambila, "mchoke munthu uyu, iye mtima mkazuzu."9Nayo adamuncha, "jina lako ndi yani?" Nae wadayanka, "jina langa ndi Legioni, pakuti tili ambili." 10Adamtondozancho ndi siwadapeleka kubwalo kwa mkoa.11Chipano kundi lalikulu la nguruwe lidali limajhe chedwa pamwamba pa phili. 12Nao adamtondoza,adakamba,tutume kwa nguruwe tulowe mkati mwao. 13Kwachimwecho wadatamula mtima ikazuzu idachoka ndikulowa mkati mwa nguruwe,nao adatawa pa nchi paphili mpaka kunyanja,ndi pafuphi nguruwe elfu ziwili zadabila mnyanja.14Ndiwajha adali amajhechela nguruwe adathawa ndikuchocha nkani ya ichochikachokela katika jiko ndi katika nchi. 15Ndeyapo wanthu ambilia dachoka kupita kupenya ichochachokela. Ndiyapo adaja kwa Yesu ndi adamuona muntu uyowapagawa ndi mapepo uyowadali ndi jeshi wadakhala panchi, wavekedwa, ndi wadali katika njelu yake timamu, nao adaopa.16Anyiwajha adali adapenya icho chodachokela kwa muntu uyowadali wapagawa ndi mapepo adamkambila ichochidachokela kwake ndi kuhusu nguruwe. 17Nao adayamba kumtondoza wachoke katika mkoa wao.18Ndi yapo wamalowa mkati mwa bwatho, munthu uyowali wapagawa ndi mapepo adamtondoza kuti wapite palimoji nae. 19Nampho siwadamuyamike nampho adamkambila, "mapita kukomo kwako, ndi kulanthu wako, ndi uwakambile. Wadakuchitila ambuye, ndi rehema uyowakupacha." 20Kwa chimwecho wadapita ndi wadayamba kuthangaza vinthu vavikulu ambavo Yesu wadachita kulake katika Dekapoli, ndi kila mmoji wadazizwa.21Ndi nyengo Yesu yapowadayombokancho upande wina. Mkati mwa bwatho, guru lalikulu lidakusanyika kumzungulila, yapowadali pamphepete pa nyanja. 22Ndi mmoji w2achogoza wa kanisa, uyowamatanidwa yairo, wadaja, ndi yapoadamuona, wadagwa ndo mwake. 23Adamtondoza kupunda ndikupunda, adakamba, "mwali wanga wamng'ono wakalibia kua. Nikutondoza, majha ndi uike manja yako pamwamba pake ili kuti wakoze kupheza aya ndi kulama." 24Kwachimwecho wadapita pamojinayo, ndi gulu lalikulu lidamchota nalo adamjala pafuphi adamzungulila.25Kudali ndi wamkozi ambae mwazi wake udali umachoka kwa vyaka kumi ndi viwili. 26Wadazunjika kwa basi phanji pa matibabu ya mbili ndi adamtuma kila chinthu ichowadalinacho. Ata chimwecho siwadapheze chalichojhe, nampho pambuyo kwake wadazidi kukala ndi khali yoipa. 27Wadavela kuhusu Yesu, chimwecho wadaja kumbuyo kwake nyengo wadali niwaenda mkati mwa gulu, nae wadagaya vazi lake.28Pakuti wadakamba, "ngati siniyagaye mavazi yake tu, sinikale wamoyo." 29Yapo wadamgafya, kuchoka mwazi kudasia, ndi wadajiela katika ntup lake kuti wadalama kuchoka kumavuto yake.30Ndi gafla Yesu wadagundua mkati mwake mwene mphavu zamchoka ndi wadang`anamka ukundi uku katika guru la wantu ndi kuuncha, ndi yani uyowaligafya chivalo changa? 31Opuzila wake adamkambila, "upenya gulu lino la kusonga likuzungulila, nawe ungokamba, ndi yani uyowanigafya?" 32Nampho Yesu wadapenya ukundi uku kupenya ambayo uyowadali wachita ichi.33Wamkazi, wadajiwa ichochachokela kwake, wadaopa ndi kutentemela. Wadaja ndi wadagwa phanchi mchogolo mwake ndikumkambilanuzene onche. 34Wadakamba kwake, "mwali, chikhulupi chako cha kuchita ukale wamoyo. Mapita kwa chikulupi ndi ulame kuchoka kumavuto yako."35Yapodali wamakamba, baadhi ya wanthu adaja kuchoka kwa ochogoza wa masinagogi amakamba, "mwali wako wafa. Chiuko chanji kuendelela kumcha mpuzisi?"36Wadakamba, "Aba, baba, vinthu vochekwa ko vikhozekana nichochele chikombe ichi. Nampho osati kwa mapenzi yanga ila mapenzi yako." 37Wadabwela ndi kuwapheza agona, ndi wadaakhambila Petro, "Simoni, bwa wagona? Siudakhoze kukesha ata ntawi imoji?" 38Keshani ndi mphemphe kuti msidaja kulowa mmayeso, kweli roho ni radhi nampho tumphi ni dhaifu.39Wadapitancho ndikupempha ndi wadatumia mau yayaja. 40Wadajancho wadaapheza agoza, pakuti maso yao yadili yolemela ndi siadajhiwe chiyani cha kumkambila. Wadaja mara ya katatu ndi kwakambila, "mkati kugona ndi kupumulila?Itosha ntawi yaika, penya"41Wadaja mara ya katatu ndi kwaakambila, "mkati kugona ndi kupulila? Itosha ntawi yaika, penya, yujha mmanja mwaachinawene dhambi." 42Ukanitieni penya yujha walipafuphi. 43Kwaakandila mphavu ndi mphawi mpe yujha chakudya.

Chapter 6

1Ni wadachoka pamenepo ni kupita kumbwani kwao, ni opuzila wake adamchata. 2Sabato yapo idafika, wadayamba kwayalua katika nyumba ya mapemphelo. Wanthu ambili adamvela ni adadabwichidwa. Adakamba wapata kuti mayaluzo yaya? "Ni njelu zanji ii wapachidwa?" "wachita bwanji malangizidwe yaya kwa manja yake?" 3"Bwanji uyu osati yuja setemata, Mwana wa Mariamu m'bale wao achi Yakobo, Yose, Yuda ni Simoni? Bwanji anyadada wake siakakala pambano pamoji ni ife?" Ni siadakondezedwe ni Mpulumusi.4Mpulumusi wadakambila, "Mlose siwakosa ulemu, ikapanda katika muji wake, pamoji ni abale wake ni apakomo lake." 5Wadakoze kuchita vodabwicha pamenepo, ila wadaikila manja odwala ochepa ni kwalamicha. 6Wadabwichidwa kupunda kwa ndande ya usakulupalila wao. Pambuyo wadaviendela vijiji va pafupi kwa yaluza.7Wadatana anyiwaja opuzila kumi ni awili wadayama kwatuma awili awili. Wadacha malamulo juu ya mizimu yoipa. 8Ni kwalamula asatenga chalichonche yapo apita ila chiboko tu. Asatenga mkate, wla chikwama wala ndalama mtumba. 9Nampho avale viatu ila osati kanzu ziwili.10Ni wadakambila, "nymba yaliyonche mulowe, kalani pamenepo hadi yapo simchoke. 11Ni muji walionche yapo siukululandilani wala kukuvechelani, chokani kwao, kung'unthani lifumbi la myendo yanu, ikale chizindikilo kwao."12Nao adapita ni atangaza wanthu alape ni kusia machimo yao. 13Adatopola mizimu yoipa yambili, wadapaka mafuta odwala ni kwalamicha.14Mfumu Herode yapo wadavela yameneyo pakuti jina la Mpulumusi lidali lajulikana kupunda. 15Akumoji adakamba, "Yohana mbatizaji wahyuka ni kwa ndande imeneyo, ii mphavu ya malangizo ichita nchito mkati mwake." Akumoji wao adakamba, "uyu ni Eliya," "akali wina adakamba, "uyu ni mlose, ngati mmoji wa anyiwaja olosa akale."16Nampho Herode yapowadavela yaya wadakamba, "Yohana nmdula mutu wahyuka." 17Chifuko Herode mwene wadalamula Yohana wagwilidwe ni wadammanga kundende kwa ndande ya Herodia (mkazake wa mkulu wake Filipo) chifuko iye wadali wamkwata.18Chifuko Yohana wadamkambila Herode, "osati bwino kumkwata wamkazi wa mkulu wako. 19"Nampho Herode wadayamba kumuipila ni wadali wafuna kumpa, nampho wadakoze. 20Chifuko Herode wadamuopa Yohana, wadajiwa kuti ni wa haki munthu oyela, ni wadamsia bwino. Ni yapo wamaendekela kumvechela wadandaula kupunda, nampho wadasekelela ni kumvechela.21Ata yapo adafika muda udapangidwa idali yawandikila yobadwa HerodeHerode wadaandalia maofisa wake sherehe, ni makamanda, niochogoza Akugalilaya. 22Ndo yapo mwali wa Herodia wadalowa i kuvina pachogolo pao, wadamsekecha Herode ni alendo adakala muda wa chakujacha ajulo. Ndo yapo mfumu wadamkambila mwali, "nipempha chalichonche uchifuna nane nikupache."23Wadamuahidi ni kukamba, "chalichocnche icho unipemphe nikupacha, ata nusu ya ufumu wanga." 24Wadachoka kubwalo wadamfuncha mama wake, "nipemphe chiani?" Adakamba, "mutu wa Yohana mbatizaji." 25Ni muda umweo wadalwa kw mfumu wadayamba kukamba, "nifuna unipachile mkati mwa m'bale, mutu wa Yohana mbatizaji."26Mfumu waandaulichidwa kupunda, nampho kwa ndande ya lapilo lake ni ndande ya lendo, wadakoza kumkanila pempho lake. 27Chimwecho, mfumu wadatuma asilikari kati ya olinda wake ni kwatuma kupita kumtengela mtu wa Yohana. Olinda wadapita kumdula mutu wali kundende. 28Wadaupeleka mutu wake mbale ni kumpacha mwali, ni mwaliwadapacha mama wake. 29Ni opuzila wake yapo adavela yameneyo, adapita kuliteng tupi lake adapita kulizika mkaburi.30Ni opuzila, adakusanyika pamoji pachogolo pa Mpulumusi, adamkambilile yonche ayachita ni kuyaluza. 31Nae wadamkambila, "majani achinawene pamalo pa sili ni tu pumulile kwa muda." Wanthu ambli adali afika n kuchoka, ata siadapate malo ya kuja. 32Chimwecho adakwela maboti adapita pamalo pa sili paoka.33Nampho wadaona nachoka ni ambili wadajiwa, kwa pamoji adatamanga kwa myendo kuchoka kumiji yonche, nao adafika kabla ya anyiio. 34Yapo adafika kumtunda adaona gulu lalikulu ni wadalengela lisungu, kwa ndande adali ngati mbelele zilibe owesa. Ni wadayamba kwayaluza vinthu vambili.35Muda yapo udaendekela kupunda, opuzila adamjela adamkambila, "pano ni pamalo pasiri ni muda wapita. 36Walaile apite miji ya jirani ni vijiji dala akajigulile vakuja.''37Nampho wadayankha, ni kukamba, "apache ni anyiimwe chakuja." Adakambila, "tikoze kupita kugula mikate ya gharama ya dinari mia mbili ni kwapacha aje." 38Wadakambila, "muli ni mikate ingati? Pitani mkapenye." Yapo adapata adamkambila, "mikate isano ni nchomba ziwili."39Wasalamulila wanthu akale katika magulu pamwamba pa matengo yawisi. 40Wadakazika katika magulu, magulu ya mamia kwa hamsini. 41Baadae wadatenga mikate isano ni nchomba ziwili, ni kupenya kumwamba, wadailapila pambuyo wadapacha opuzila wake pachogolo pa gulu. Ni pambuyo wadagawa nchomba ziwili kwa wanthu onche.42Adaja onche nipaka adakuta. 43Adakusanya vipande va mikate idakala, vidajala vikapu kumi ni viwili, ni ata vipande va nchomba. 44Ni adali wachimuna elu zisano adaja mikate.45Pamwepo wadakambila akwele mmaboti apite malo ina, mpaka Bethsaida, muda uje ni walaila wanthu. 46Yapo adali atochoka wadapita kupili kupempha. 47Yapo kudali ujulo ni maboti yao muda umeneo yali pakati kati ya nyanja, nae wadali yoka kumtunda.48Yapowadaona avutika kuguza nkhati kwandande ya mphepo idasaucha. Yapo udawandikila umawa wadachota, waenda pamwamba pamaji, ni wadauna kwapita. 49Nampho yapoadamuona waenda pamwamba pa maji, adalowedwa ni wasiwasi ni aganiza mzimu daadi adabula pokoso. 50Kwa ndande amuona adali kuopa mara wadakamba na wadakambila, "mukale ojikulupalila! Ni ine msakala ni mantha."51Wadalowa mkati mwa boti, ni mphepo idasia kuputa, nao adazizwa kupunda. 52Chimwecho adali adaelewe mate ya ija mikate. Chifukwa njelu zao zidali ni uelewa waung'ono.53NAo yapo adayomboka kuchija, adaika muji wa Wagerasi maboti yadabiza ndondowe. 54Yapoadachika mmaboti, gala adamjiwa. 55Adatamanga kutangaza muji onche ni adayamba kwapeleka odwala kwa machela, kila yapo adavela wakuja.56Paliponche wadalowa katika vijiji au miji au katika nchi, wadaika odwala pamalo pali msika, ni adampempha waruhusu kugusa mkunjo wa nchalu yake. Ni onche adamgusa adalama.

Chapter 7

1Afarisi ndi otembela wina amachokhela Kuyerusalemu adasonkhana kukambana ndi iye. Adaona kuti omphuzira wake akumojhi amadya mikate mmanja mosasambe.2Adaonakuti omphuzira wake akumojhi amadya mikate mmanja mosasambe. 3(Afarisayo ndi Ayahudi onche sakudya ngati sadasambe manja yao bwino. 4Afarisayo ngati achokela kumsika sakudya mbakana asambe huti. Ndi kuli malamulo yina ayachata, ngati kuchuka vikho, miphika ndi vyombo va ziwiya, ndi mipando iyo atumikila nyengo ya chakudya.)5Afarisi ndi amphuzisi amalamulo adamuncha Yesu, ndande chiyani omphuzira wauosasunga mwambo wa makolo wao wadaasiila ndande chiyani akudya nkate popande kusamba mmanja?''6Nampho iye wadaakambila, Isaya wadakamba bwino pakati panu achiphamaso, wadalemba wanthu anyiyawa anilemekeza pakamwa pao nampho mitima yao ili patali ndiine. 7Anichitila phembezo lopande mate, ayaluza na malamulo ya wanthu ngati malandilidwe yao.8Mwasia lamulo la Mulungu ndi kugwililila miyambo ya wanthu. 9Ndi wadakambila,mwakana chitema lamulo la Mlungu kuti msunge miyambo yanu. 10Pakuti Musa wadakamba mlemekezetate wako ndi mai wako,ndi uyo waakamba kuipha atate wake kupima amake mmeneyo siwafe.'11Nampho mkamba,ngati munthu wakakhamba kwa atate wake kapima kwa amake mtandizo walionche mkadalandila kuchokela kwaine. 12Kwaicho siumvomeleza kuchita chilichonche kwa atate wake akapima amani wake. 13Mchita lamulo la Mulungu kukhala lopandi mati pakuphilika miyambo yanu, ndi mchita vintu vambili vamtundu umeneo.''14Wadaatanancho wanthu ndi kwakambila anyaimwe mwaonche msadanivela ine,ndi mvanenavo. 15Palibe chalichonche kuchokela kubwalo kwa munthu icho chikhoza kumdicha munthu yapochilowa kwaiye.Ikapande icho chimchoka munthu ndeicho chimdecha. 16(Penyelelani mzele uwu,ngati munthu waliyenche wali ndi makutu yovela ndi wavele).17Yesu yapo wadaasiya wanthu wadalowa mnyumba, omphuzira wake adamfuncha pakati pa fanizo limeneli. 18Yesu wadakamba, ndi anyaimwe namwe mkali osavanenavo? Simjhiwa kuti chalichonche chilowa kwa munthu sichikhoza kumdecha. 19Ndande sichikhoza kupita kumtima wake, nampho chilowa mmimba mwake ndikupitilila kuchumbujhi Pakati pa mau yaya Yesu wadavichita vakudya vonche kukhala voyera.20Wadakamba, "chijha chimchokha munthu ndeicho chimdecha. 21Ndande chichokha mkati mwa munthu, kubwalo kwa mtima, kuchoka maganizo yoipa chiwelewele, kuba ndi kuphana. 22Chigololo, khumbilo loipa, kuipa mtima, unami, kunyasanyasa, kujinyozanyoza, kupusa. 23Voipa vonche ivi vichoka mkati, ndeivo vimdecha munthu."24Wadanka pajha ndikuchoka kupita kudera la Tiro ndi Sidoni. Wadalowa mkati ndisiwadaune munthu waliyonche, wajhiwe kuti wadali pamenepo, nampho siwadakhoze kubisika. 25Nampho mwazizi wamkazi, uyo mwana wake wa mng'ono wadali ndi mzimu oipa, wadavela nkhani zake, wadajha, ndikughwa mmyendo mwake. 26Wamkazi mmeneyo wadali wa Kuyunani, wa mtundu wa Kifoiniki. Wadamphempha iye wautopole mzimu oipa umchoke mwana wake.27Yesu wadamkambila wamkazi, "asiye wana adyechedwe huti, pakuti osati zene kutenga nkati wa wana kwa ataila agalu." 28Nampho wamkazi wadayankha ndi kukamba, "etu Ambuye, ingakale agalu panchi pa tebulo akudya manyeyeko ya chakudya chawana."29Wadamkambila, pakuti wakamba chimwecho, mapita. Mzimu oipa wamchoka mwana wako. 30Wamkazi wadabwela kukhomo lake ndi kumkhomana mwana wake wagona pachikha, ndi mzimu oipa udali wamtuluka.31Yesu wadachoka kubwa la dera wa Tiro kupitila Sidoni kupita kunyanja ya Galilaya mbakana kudera la Dikapolisi. 32Adampeleka munthu wadali gontha ndi siwakhoze kukhamba bwino, adamphempha Yesu kuti wamuikila manja.33Wadamtulucha kubwalo kwa gulu kwa kubisika, ndi kuika vyala mmakutu yake, ndi pambuyo polavula malovu, wadamgunda lilime lake. 34Wadapenya maso kumwamba, ndi kujhuma ndi kumkambila, Efatha, kunena kuti masuka. 35Nyengo imweyo makutu yadamasuka,ndicho chidachekeleza lilime chidawanangidwa ndi wadakhoza kukamba bwino.36Ndi wadaalamu asamkambila munthu waliyonche nampho umowadaalamulila, ndeumo amalengeula nkhani izo mwaunyinji. 37Zene kuti adadabwa, ndi kunena wachita kila chinthu bwino. Wachita magontha kuvela ndi osakambe kukamba.''

Chapter 8

1Kupitila siku zimenezo, kudalincho ndi gulu lalikulu, ndi adalibe ndi chakudya. Yesu wadatana opuzila wake wadakambila, 2"nilionela lisungu gulu ili, aendekela kunkala nane kwa siku zitatu ndi alibe chakudya. 3Nikatawanya ajibwela mmakamo mwao bila kudya ankoza kuzimia mnjila mwa njala. Ndi baadhi yao achoka patali sana." 4Opuzila wake adajibu, "situpate kuti mikate yatosha kwakunticha wanthu anyiwaya pamalo yapo pasiidwa?"5Wadafuncha, "mli ndi vipande vingati va mikate?" Adakamba, "saba." 6Wadaramula gulu linkale panchi, wadatenga mikate saba, wadayamikila ndi kutyola wadaninka opuzila wake aiike pachogolo pao, naoncho adaiika pachogolo pa gulu.7Nampho adali ndi nchomba zazing'ano zidukuduku, ndi baada yoyamikila, wadalamula opuzila wake waagawile ndi vimenencho. 8Adadya ndi adatosheka, ndi adakusanya vipande ivo vidankalila, vikapu vavikulu saba. 9Adankalibia wanthu elfu zinai, ndi wadasia ajipita. 10Ndipo wadalowa maboti ndi opuzila wako, nin adapita pakati pa Dalmanuta.11Ndipo Afarisayo adachoka kubwalo ni kuyamba kubishana naye. Adauna waninke chiwalilo kuchoka kumwamba, kwakumuesa. 12Wadaganizila kwa patari mutima mwake wadakamba, "ndande chiyani chibazi ichi chiunauna chiwalilo? Nikukambilani anyiimwe uzene, palibe chiwalilo sichinchachedwe kwa chibaziichi." 13Ndipo wadasia, wadalowa mkati mwa batincha, wadachoka kuelekea bendeka lina.14Nyengo imeneyo opuzila adayawalila kutenga mikati. Adalibe mikate zaidi ya chipande chimoji ichochidali m'boti. 15Wada anya ni kukamba, "mnkale masa ni mjilinde dhidi ya vichito vya Mafarisayo ni vichito va Herode.16Opuzila adakambilani, anyiiwo kwa anyiiwo, ndande tulibe mikate." 17Yesu wadajiwa limenelo, ni wadakambila, ndande chiyani mkambana kuhusu kuto kunkala ni mikate? Simdajiwe bada? Simuelewa? Mitima yanu yankala ya chisanga?18Muli nimaso, simpenya? Muli ni makutu, simbvela? Simkumbuka? 19Yapo nidaigawa mikate isano kwa wanthu elfu tano, ,datenga vikapu vingati ivo vidajala vipande va mikate? Adamjibu, "kumi ni viwili."20"Ndi yapo nidaigawa mikate saba kwa wanthu elfu zinai, mdatenga vikapu vingati?" 21Adakamba, "saba." Wadakambila, "bado simuelewa?"22Adaja Bethsaida wanthu achameneo adampeleka adampeleka kwa Yesu munthu siwapenya, ni adampempha Yesu wamguse. 23Yesu wadamgwila kwa jancha yuja siwapenya, ni kumchogoza kubwalo kwa kijiji. Yapo wadalavula malovu pamwamba pa maso yake ni kuonyosha mancha yake pamwamba pake, wadamuncha, "uona chalichonche?"24Wadapenya kumwamba ni kukamba, "niona wanthu aonekana ngati mitengo iyenda." 25Ndo wadanyoshancho mancha yake pamwamba pamaso yake, munthu yujha wadachakula maso yake, wadaonancho, ni wadaona kila chinthu chabwino kila chinthu chabwino. 26Yesu wadamsiya wajipita kukoma ni wadamkambila, "siudalowa kumjini."27Yesu wadachoka ndi opuzila wake kupitila vijiji va Kaisaria ya Filipi ya yapo adali nchila wadauncha opuzila, "wanthu akamba ine yani?" 28Adajibu adakamba, "Yohana abatiza," wina adakamba, "Eliya ndi wina, mmoji wa olosa."29Wadamuncha, "nampho anyiimwe mnkamba ine ndi yani?" Petro wadamkambila, "iwe ndi Kristo." 30Yesu wadamkaniza sadamkambila munthu waliyenche kumuhusu iye.31Ni wadayamba kuwayeruza kuti mwana wa mwanadamu lazima wateseke kwa vinthu vambili, ndi siwakanidwe ndi viongozi ndi wakulu anchembe ndi olemba, ndi siwapedwe, ndi baada ya siku zitatu siwahyuke. 32Wadakamba yameneyo kwa uwazi. Ndeyapo wadamtenga Petro pamphepete ndi kuyamba kumkalipila.33Nampho Yesu wadang'anamuka ndi kwapenya opuzila wake ndi kumkalipila Petro ndi kukamba, "pita kumbuyo kwanga Satana! Siujali vinthu va Mulungu, nampho vinthu va wanthu!" 34Ndeyapo wadatana gulu ndi opuzila wake pamoji ndi kuakambila, ngati kuli munthu wauna kunichota wajikane mwene, watenge mtanda wake ndi wani nchate.35Pakuti waliyonche wauna kuyalamicha maisha yake siwayataize, ni waliyonche uyosiwayataile maisha yake kwa ajili ya mau la Mulungu, siwayalamiche. 36Imtangatila chiyani, munthu kupatajika lonche, ni badae kupata hasala ya maisha yake? 37Munthu wamkoza kuchoncha chiyani badala ya maisha yake?38Waliyonche wanionela rohoni nchani ni mau yanga kupitila kibazi ichi cha chimolemole ni chibazi cha anyiyawa achima, mwana wa mwanadamu siwamwonele nchani yaposiwaje pakati pa uumu wa atate wake pamoji ni angelo oyela.

Chapter 9

1Ndi wadakamba kwao, "uzene ndikamba kwanu, ochepa wanu kuli wandu yao aima yapa salawa nyia pambuyo popenya uulu wa Mulungu ndi ubwela kwa mphavu." 2Ndi pambuyo pasiku sita, Yesu wadatenga Petro, Yakobo ndi Yohana pamoji ndi iye kupili, oka ndiposo wadayamba kubinda pakati pao. 3Vovala vake vidayamba kuwala kupunda, voela kuposa uyowalicha walionje pajiko.4Ndiposo Eliya pamoji ndi Musa adachoka pachogolo pao, ndadali ndakamba ndi Yesu. 5Petro wadayankha ndikukambila Yesu, "Mpuzisi ndi chabwino ie kukala pano, ndi timange vibanda vitatu, chimoji ndande yako, ndi chimoji ndande ya Musa ndi china cha Eliya." 6(Pakuti siwadajiwe chiyani cha kamba, adaopa kupunda.)7Mitambo idachokela ndi kwavinikila. Ndiposo mau yadaveka mmitambo imakhamba, "uyu ndi mwanawanga, ndimkonda. Mvecheleni iye." 8Chizulumikilo, yapo adali ndapenyana, sadamuone walionje pamoji ndi anyiiwo, ndipo Yesu pe.9Yapo adali ndiachika kuchoka kupili, wadalamula siwadakambila wandu chilichonje icho adachiona mbaka mwana wa Adamu yapo siwauke kuchoka kunyifa. 10Ndiposo adayasunga vindu vao achinawene. Nambo amakambilana anyiiwo kwa anyiiwo ndi chiyani mate yake, "kuuka kuchoka kunyifa''11Adamuncha Yesu, "pandande iti olemba lazima Eliya waje huti?" 12Wadakambila, "uzene Eliya siwabwele huti kulamicha vindu vonje. Pandande iti walembedwa mwana wa Adamu lazima wapeze mateso yambili ndi waipidwe? 13Nambo nikamba kwanu Eliya wadatobwela, ndi adamchita ngati umoadaunila, ngati muja malembo yadalemba kuhusu iye."14Ndeyapo adabwele kwa opuzila, adaona wandu ambili wazungulila ndi Masadukayo amakangana nao. 15Ndipo yapo adamuona, chigao chonje chidadabwa ndikumtamangila kumlonjela. 16Wadamfunja opuzila wake, "mpikisana nao pamwamba pachiyani?"17Mmoji wao pakundi adamuyankha, "mpuzisi, ndidampeleka mwana wanga kwanu, wali ndi chiwanda choipa ambacho chimtita siwadakoza kukamba, 18ndi kumchiticha mtendemela ndikumgwechapaji, ndikuchoka tovu mkamwandi kukhaya mano ndi kulimba, ndidapempha opuzila wanu kumchocha chiwanda, nambo adalepela." 19Adayankha, "chibadwa, chosakulupilile, sindikale namwe kwandawi yanji? Sinditengelane namwe hadi chakonji? Mpelekani kwanga."20Wadampeleka mwana wake. Chiwanda chidamuona Yesu, chizulumukilo wadamtila potendemela. Wadagwa panji ndi kuchocha tovu mkamwa. 21Yesu wadamfunja atate wake, "wadalipahali iyi pandawi yanji?" Atate adayakha, "choka umwana. 22Ndawi ina wakugwa pachoso au mmaji, ndi kuyesa kumpa. Ngati mukoza kuchita chita chilichonje mutukululukile ndi mututangatile."23Yesu wadamkambila, "ngati uli tayari? Kila chindu chikozekana kwa walionje wakulupilila." 24Chizulumukilo tate wamwana wadalila ndi kukamba, "ndavunanavo! Nitangatile kuto kuvananavo kwanga." 25Ndawi Yesu ndiwaona msongano utamangila kwao, wadamkalipila chiwanda choipa ndikukamba, "iwe chiwanda chosakambe ndi gonda, ndikulamula msie, usidalowanjo kwaiyenje."26Wadalila kwa mbavu ndi kumsakalicha mwana ndi chiwanda chidamchoka. Mwana wadaonekana ngati waa, ndipo ambili adakamba, "wafa" 27nambo Yesu wadamtenga kwa janja ndikumuucha, ndimwana kuima.28Ndawi Yesu walowa mnyumba, opuzila wake adamusa chisisi, "ndande yanji, sitidakoze kuchocha?" 29Wadakambila, "pandande iyi sichichoka bila mapempelo."30Adachoka paja ndikupita Kugalilaya. Siwaune mudu waliyonje wajiwe kuti ukowapita, 31pakuti wamayaluza opuzila wake. Wadakambila, "mwana wa Adamu siwaikiche mmaja mwa wandu, ndi sampe. Yako siwakale waika, baada ya siku zitatu suwaukenjo." 32Nambo sadavane navo mau yaja, ndi amaopa kumfunja.33Ndipo adaika Kapernaumu. Ndawi wali mnyumba wadaunja, "mmakambana chiyani ndawi muli njila?" 34Nambo adakala osayakhe. Ndipo adali ndi akangana mnjila kuti yani wadali wamkulu kuposa. 35Wadakala panji ndikwatana kumi ndawili pamoji, adakamba nao, "ngati walionje wauna kukala oyamba, ndikuti wakale otela ndi kutumidwa ndi wandu woje."36Wadamtenga mwana wang'ono ndi kumuika pakati pao. Wadamtenga pamanju pake, ndikukama, 37"waliyonje wamlandila mwanayu pajina langa, wanilandila ine, ndi ingakale mundu wanilandila, siwanilandila ine pe, nambo piya uyowanituma."38Yohana wadamkambila, "mpuzisi tidamuona mundu wachocha chiwanda pajina lake ndi tidamkuniza, pandande siwatuchata." 39Nambo Yesu wadakamba, msidamkaniza, pakuti palibe uyosiwachite njito yaikulu pa jina langa ndiposo pambuyo wakambe mau lalilonje loipa pamwamba panga.40Walionje wali sawa ndi ie wali upande watu. 41Walionje uyo siwakunikhe chikombe cha maji ya kumwa pandande uli ndi Kristo, uzene ndikukambilani, siwasoweza haki yake.42Walionje wakulakwilani yawa wana anikulupilila ine, idakakala bwino kwake kumangidwa mwala wa msingi mkosi ndi kutaidwa kunyanja. 43Ngati njaja lako likakulakwila udule ndi mbasa kulowa pakati pa uumu bila janja kuposa kulowa malamulo ulindi manja yonje pamoto, "uwosiutima." 44(Chatilila mstari iyi, "pamalo yapo tekenya sakua ndi moto uliosiutima." Siuli pa nakala za kale).45Ngati mwendo wake ukakala kusila, uchile ndi bwino kwako kulowa uumu ukakala ndi chilema, kuposa kuponyedwa mmalamulo ndi nywendo iwili. 46(Penyelela; mstari huu, "pamalo yapo tekenya siwakua ndi mto uwo siukoza kuti mau" siulipamalo paufumu wakale).47Ngati diso lako lakulakwila lizule, ndi bwin kwako kulowa kuufumu wa Mulungu uli ndi diso limoji, kukala ndi maso yawili ndi kutainidwa kuzimu. 48Pamalo pali nditekenya yao sakua, ndi moto uwo siutima.49Pakuti kila mmoji siwakwelezedwe moto. 50Mchele ndi wa bwino, ngati mchele ukasoweza kukoma kwake, uichitenji ikale ndi.

Chapter 10

1Yesu wadachoka malo yameneyo wadapita kumkoa wa Wayahudi ndimalo yachogolo la mchinje Yorodani ndi wanakanyinji adamchatancho. Wada ayanezancho ngati mmene udali mtete wake kuchita. 2Asomisomi adaja ndi ku muyesa ndi adamuncha, "pali bwino wammuna kusiana ndi mkazake?" 3Yesu wadaayanka, "Musa wadakulamulani chiani?" Adakamba, 4"Musa wadalamula kulemba chipaso chakusiana ndipambuyo kumtopola wamkazi."5Chifuko chimitima yanu yolimba ndiye chifukwa chake wadakulembelani lamulo limenelo. 6Nampho kuchokela chiyambo cha makonjedwe munengu wadaakonja wamuna ndi wamkazi.'7Chiuko chaichi wamuna siwamsiye tata wakendi mayi wakendi saakalile limoji ndi mkazake. 8Ndi achameneo siakale tupi limoji chiuko osati awilincho ikapanda tupi limoji. 9Kwammwecho chimenene walilunjizana mumengo muntu siwadachi siianicha.''10Yapo adali mkati mwa nyumba opuzila wake adamuncha kupitira ili. 11Wadaakambila, "waliyonche wamsia mkazake ndikukwatira wamkazi mwena wachita chitole kupitila iye. 12Wamkazi nayenche wakamsia mmunake ndi kukwatiwa ndi wammuna mwena wachita chitole."13Naoncho adampelekela wana waowa ang'ono ang'ono dala awatonose nampho puzila wake adaakaniza. 14Nampho Yesu yapo wadajiwa limenelo siwada sangalale nalo wadaakambila, "asiilileni wana waang'ono ang'ono aje kwaine ndi simda asiicha chiukwa alingati anyiyawa uuru wa Mulungu nde wao.15Uzene ndikukambilani, waliyenche siwadaulandila uuru wa Mulungu ngati mwana wamung'ono chazene siwakoza kulowa paufuru wa Mulungu. 16Pambuyo wada atenga wana wa ang'ono ang'ono onmarya mwake ndi kwa apacha veneleli wa kwa aikula manja pamwamba pao.17Ndeyapo wadayamba ulendo wake muntu mmoji wadamtamangira ndi kuchicha maombono yake pachogolo pake, "wadamuncha, oyaluza wa bwino ndichite chiyani dala ndikoze kupeza uuru osata?" 18Ndi Yesu wadakamba, "ndande yanji wanditana wabwino? Palije waliwa bwino ikapanda Mulungu yeka." 19Uyaji wa matauko usadapa usadachita chitole usadaba usadavemeleza mtira usadanyenga alemekeze atata wako ndi amalu.''20Muntu yuja wadakamba, "myaruzi yaya yonche ndeyatengelela kuyambila ndikali muyamata." 21Yesu wadampenya ndikumkonda, wadakambila, wasowedwa chinthu chimoji ufunika uguliche vonche ulinavo ndi wapacha wanthu otedwa ndi siukale ndi kuikala kumwamba ndi udaje kundi chata. 22Nampho wadatedwa mphavu chiuko cha chawakambidwe yameneyo wadachoka ndiwadandaula chiuko wadali ndi chuma chambili.23Yesu wadapenya malo yonche ndi kwaakambila oyaruzidwa wake mtundu wa mji siikalile kulimba owina kulowa muufru wa Mulungu. 24Oyaruzidwa adezizwa kwa mau yaya, nampho Yesu wadaakambilancho, "wana mtundu wanji umoikalila kulimba kulowa muufuru wa Mulungu! 25Kupepuka ngamia kulowa njuye la toola kupambana muntu owina kulowa muufru wa Mulungu.''26Adazizwa kupunda ndi kukambilana mmwemo yani siwapurumuke. 27Yesu wada apenya ndikukamba, "kwa muntu siingakozeke nampho osati kwa Mulungu pakati pa Mulungu yonche yakozekana." 28Petro wadayamba kukamba naye, "penya tasia vonche nditakuchata."29Yesu wadakamba uzene ndikukambilani anyaimwe pauvinje waisia nyuma nyumba kapena mlongo wake wake kapena wana kapena ntaka chiuko chaine ndi chiuko cha mau la Mulungu. 30Mmene siwalandila mtundu wa mia ndikupitilila chapano pampano pajiko nyumba mlongo wako mama wana ndi ntaka kwa mavuto ndi jiko likuya mtendele wosata. 31Nampho ambili alioyamba siakale otela ndiotela siakale oyamba.''32Adali mnjira kupita ku Yerusalemu Yesu wadaajolela mchogolo mwao oyaruzidwa adazizwa ndi anyiwaja amachata m'mbuyo adaopa. Nde pamene Yesu wadaachocha pamphepete ndiwaja kumi ndi awili ndi wadayamba kwa itaakambila chimene sichimchokele posachedwa. 33"Penya tipita Kuyerusalemu, ndi mwana wa muntu wapelekedwa kwa mapadure waukuru akuru ndi olemba si amulamule wae ndisiamchoche kwa wanthu ajiko. 34Siamchetu chipongwe siamlavulile malovu, siamtyape vikoti ndi siamupe nampo pambuyo pa masiku yatatu siwazuke."35Yakobo ndi Yohana wana wa Zebedayo adaja kwaiye ndikukamba, "mwalimu, tikufuna tichite chilichonche sitikupembe." 36Wadaakambila, "mufuru ndikuchitileni chiyani." 37Adakamba, "tilamule tikale nawe pa ufuru wako, mmoji janja la kwene mmoji janja la kumayele."38Nampho Yesu wadayankha, "simjiwancho mpempha simkoze kuchimweka maji chiko chimene sindimwele ine kapena kudikamula ubatizo umene sindibatizidwe?" 39Adamkambila, "tikoza" Yesu wadaakambila chiko sindimwele. Simchimwele ndi ubatizo umeme kwanyiwe nda batiadwa simukoze. 40Nampo suwakale janja langa lakumanjele osati ineochocha nampo kwa anjiwaja kwa inyaiwo yatokonjedwa.''41Anyiwaja oyaluzidwa wena kumi yapo adevela yameneyo adayamba kwa akwiila Yakobo ndi Yohana. 42Yesu wadatana kwaiye ndikukamba mujiwa kuti anyiwaja aganizilidwa kuti olamulila ndi wantu wao ojiwika waalangiza mala mlo pamwamba pao.43Nampo sifunika kukala nchimwechi pakati panu waliyenche siwakale wamkuru pakati panu mate wa kutumikilieni, 44ndi waliyenche siwakale oyamba pakati panu wakale kapolo waonche. 45Pakuti mwana wa muntu siwadaje kutumikilidwa ikapanda kutumikila ndi kuyachoche malamidwe yake malipilo kwawena.''46Adaja Kuyeriko; yapo wadali mkukuchoka Kuyeriko oyaluzidwa wake ni guru lawantu ambili mwana wa Timayo Batimayo kipofu mwombaji wadakala mpepete mwa njila. 47Yapo wadavela kuti Yesu Mnazareti wadayamba kubwa pokoso ndi kukamba, "Yesu mwana wa Daudi ndichitile lisungu." 48Ambili adamkanikiza kwa kumkalipila yuja osapenya ndi amkambila wakale kachete nampo wadalila kwa mau ya pamwamba, "mwana wa Daudi ndi chitile lisungu!''49Yesu wadaima ndi kulamula watanidwe, adamtana yuja osapenya ndi akamba kuti olimbikila ima, Yesu wakutana. 50Wadataya pampepete je kati lake, wadatamanga kupunda ndi kuja kwa Yesu.51Yesu wadamuyanka ndikukamba, "ufuna ndikuchitile chiyani, yuja wammuna osapenya yadamuyanka." Mwalimu ndifuna kupenya. 52Yesu wadamkambila, "mapita kurupililo lako lakulamicha pamwepo ndi pamuepo maso yake yadalama ndi wadamchata Yesu munjila.

Chapter 11

1Nyengo imeneyo yapo adajha Yerusalemu,yapo adawandikila Besthfage ndi Bethania,pa pilila mizeituni,Yesu adatima awili mwa mojhi a opunzila wake. 2Ndi kwakambila, mapitani muchijiji ichochiti wandikila ndi ife nafe yapo simlowe mmenemo,simpheze mwanepande uyo siwadakwelwedwe mmesuleni ndi mnipelekele kwanga. 3Ndi ngati waliyenche siakukambilani ndade chiyani mchita chimwechi? Mfunika kunena, wamkulu wamfune ndi mara siwambweze pano.''4Adapita ndi kumpheza mwanapunda wamangidwa kubwalo kwa komo mwa mlaga uwo wamasulidwa nawoncho adammasula. 5Ndi amojhi a wandhu yawo adaima pajha ndi adakambila, "mchita chiyani, kummasula mwana punda mmeneyo?" 6Adakabila ngati Yesu umowadakukambilani, ndi wandhu adaasiya ajhipita.7Opunzila awili adampelekela mwana punda kwa Yesu ndi adayala vovala vawo pamwamba pake dala Yesu wakoze kumkwela. 8Wandhu ambili adayala vovala vawo mnjila, ndi wena adayala ntawi izo adayadula kuchokela mminda. 9Anyi adapita kuchogolo kwa iye ndi anyiwaja adamchata adatimba mapokoso, "Hosana! Odalisidwa wakujha kwa jhina la okuzika. 10Ukuzikwidwe ufumu ubwela wa atate wake Daudi! Hosana kwa uyo walikumwamba"11Ndipo Yesu wadalowa ku Yerusalemu ndi kupita muhekaluni ndi adapenya kila kandhu. Chipanonyengo idaluyata, wadapita Bethania pamojhi ndi wajha kumi ndi awili. 12Siku idachatila, nyengo yapoadali kubwela kuchokela Bethania, wadali ndi njala.13Ndi wadaona mtengo wa vipacho uwo udali ndi machemba kwa kutali wadapita kumpenya ngati wadakakoza kupeza chalichonche mmwamba mwake. Ndi nyengo yapo wadapita kwa umeneo, siwadapeze chalichonche ikapanda machamba, pakuti sidali nyengo ya vipacho. 14Adaukambila, "palibe waliyenche siwadye chipacho kuchokela kwa iwencho." Ndi opuzila wake adavela.15Adajha Kuyerusalemu, ndiiye adalowa muhekaluni ndi kuyamba kuwachocha kubwalo ogulicha ndi ogula mkati mwa hekalu. Adang'anamula andalama ndi mipando ya anyiyawo amegulicha ghunda. 16Siadampache lamulo waliyenche kubala chalichonche muhekaluni ichochimakoza kugulichidwa.17Adayaluza ndi kunena, bwanji sidalembedwe, nyumba yanga itanidwe mnyumba ya mapemphelo kwa mayiko yonche? Nampho mwaichita jenjhe la olanda. 18Wakulua akulu anhembe ndi olemba adavela lema wadanenela, nawoncho adauna njila ya kumpha. Nampho atachimwecho adamwopa chifuko gulu lidadabwichidwa ndi mayaluzo yake. 19Ndi kila nyengo ujulo yapoumafika, adachoka mumjini.20Yapo adali mkuenda umawa adaona mtengo wa vipacho wauma mpakana mmizo yake. 21Petro wadakumbukila ndi kunena, "Rabi! Kapenya mtengo wa vipacho uwo wa uleswa wauma."22Yesu adawayankha, "mkale nde chikhulupi mwa Mlungu. 23Kulupalilani ndikukambilani kuti waliyenche walikambila pili yili, Choka, ndi ukajitaye mwewe mnyanja, ndi ngati walibe mmtima mwake nampho wakulupalila kuti ichowanena ichichokele, ndipo chimwecho Mulungu siwachite.24Kwaicho nikukambilani kila chindhu mmphemphacho ndi kufunjha chifuko cha iye, kulupalilani kuti mwalandila, ndiivo sivikale vanu. 25Nyengo yapo muime ndi kupempha, mfumuka kulekelela chalichonche mlinacho pa aliyenche, kuti ambuyanu wali kumwamba akulelekelelani naponcho anyiimwe volakwa vanu. 26(penyelelani; mzele uwu, "nampho ngatisimlekelela, iye atate wanu wali kumwamba siwakulekelelani machimo yanu." Palijemo mu mmalembo ya kale).27Adajha Kuyerusalemu ncho. Ndi Yesu yapowadali nkutenda muhekaluni, wakuluwakulu wanchembe, olemba ndi midala adajha kwaiye. 28Adamkambila, "kwa malamulo yati uchita vindhu ivi? Ndi yani wakupacha malamulo kuyachita yaya?"29Yesu wadakambila, "sinikufuncheni funjho limojhi. Nikambileni ndi ine sinikukambileni kwa malamulo yati niyachita yaya. 30Bwanji ubatizi wa Yohana udachoka kumwamba kapena udachoka kwa wandhu? Niyankheni."31Adafunchafuncha mmojhi mwao ndi kung'anamukilana ndi kunena, "ngati tikanena, "kuchoka kumwamba" siwamene kwa ndande chiyani basi simdalakulupalile? 32Nampho ngati tikanena, "kuchoka kwa wandhu," adawaopa wandhu pakuti wonche adagwilila kuti Yohana wadali mlosi." 33Ndipo adamuyankha Yesu ndi kunena, "sitijhiwa." Ndipo Yesu adakambila, "ingakale ine sinikukambilani ndi kwa malamulo yati niyachita yochita yaya.

Chapter 12

1Ndipo yesu wadayamba kuayaluza mwa chianizo wadakamba munthu wadavyala muunda wa mizabibu wadazunguzila seli ndi kukumbajenje lovundikila mwinyo wadamanga mnara ndi kulipangi cha hayara kwa alimi mizabibu ndi kupita ule ndo wapatali. 2Nthawi yapo idafika wadamtuma mtumiki kwa alimi amizabibu kulandila kuchoka kwa anyiiwo vipacho vamunda wa mzabibu. 3Nampho adamgwila ndi kumbula ndi kumtopola popande chilichonche.4Wadamtuma mtumiki mwina, adamvulicha kumutu ndi kumchita vichito va nchoni. 5Wadamtuma mwinancho, uyu mmoji adampa, adaachitila wina ambili vichito ngali vimwevo, amaabula ndi wina kuapa.6Wadali wakali ndi munthu mmoji wa kumtuma mwana wa chikondi. Iye wadali otela uyo wadatumidwa kwa anjiiwo, ndi wanena samlemekeze mwana wanga. 7Nampho opanga hayaya adakambichana, "achinawene ndi kusiilidwa sikukakale kwatu."8Adamgwila ndi kumpa ndi kumtaya kubwalo kwa munda wa mizabibu? 9Kwaicho bwa siwachite chiyani mwene munda wa mizabibu? Siwaje ndi kuapa alimi a mizabibu ndi kuapacho wina mundao.10Simdasome lembo ili? Mwale adaukana omanga wakale mwala wa pamphepete. 11Ichi chachoka kwa Ambuye ndi chodabwicha pamosa patu. 12Adafuna kumgwila Yesu nampho adaopa gulu la wanthu adaiwa kuti chifanizo wachikamba chifukwa cha amnyiio kwa icho adachoka ndi kumsuya.13Adafuna kumgwila 14Yesu nampho adaopa guhila warithu, adajiwa kuti chifanizo wachikamba chifukwa cha anyiiwo, kwa icho adachoka ndi kumsija, ndipo adaatuma akumoji amafarisayo ndi Maherode kwa iye kuti akamchele kwa mau. 15Yapo adafika adawamkambila, Apuzisi tijiwa kuti siuvela va munthu, waliyenche ndi siulangiza kukonda akumoji pakati pa wanthu, uyaluza njila ya Mulungu mwa uzene, bwa ndi malinga kusonkha kapena noto."16Adampeleka imoji kwa Yesu, wadakambila, "bwa! nkhope ndi malembo yani yapandi yayani?" Adakamba, "ya Kaisari." 17Yesu wadaakambila, mpacheni Kaisari vinthu va Mulungu adadabwichidwa ndi iye."18Ndipo Masadukayo anyiwaja akamba palibe chizukililo adampitila ndi kumfuncha, kuti, 19"apuzisi, Musa wadatilembela kuti ikakala munthu wafa ndi wamsiya wamkazi popande mwana m'bale wake wamtenge wam'bale wakeyo kuti wakampatile wana m'bale wake."20Kudali abale saba, oyamba wadakwatila mkazi ndi kufa asiwadasiye wana. 21Ndi wakawili wadamtenga naye wadafa siwadasiye mwana, ingakale wa katatu naye. 22Ndi wa saba wadafa siwadasiye wana potela ndi wamkazi wadafa. 23Nyengo ya chizyukililo, yaposahyuke bwa! Siwakale wamkazi wa yani? Ndande achiabale onche saba adali achiamunake.24Yesu wadaakambila ichi osati ndande mwasowezedwa ndande simjiwa malembo ndi mphavu za Mulungu? 25Nyengo yohyuka kuchoka kwa akufa palije kukwata palije ku kulowa m'banja, wanthu saakale ngati angelo akumwamba.26Nampho kukuza akufa yao sahyushidwe, bwa! Simdasoma kuchoka chikalakala cha Musa, mu nkhani ya fukutu, Mulungu umowadakamba ndi kumkambila, "Ine ndi Mulungu wa Abraham, ndi Mulungu wa Isaka ndi Mulungu wa Yakobo?" 27Iye asati Mulungu wa akufa koma amoyo ndi zoona mwasowa.''28Mmoji wa olemba wadaja ndi kuvechela machezelo yao wadaona Yesu waayankha bwino, wadamfuncha bwa! Ndi lamulo liti lili lili lalikulu ndi loyamba kupunda yonche? 29Yesu wadamuyankha "yoyamba ndi ili. "Vechela Israeli, Ambuye Mlungu watu, Ambuye ndi mmoji. 30Mkonde Ambuye Mulungu wako kwa mtima wako onche, kwa njelu zako zonche ndi kwa mphavu zako zonche. 31Lamulo la kawili ndi ili mkonde wa pafupi wako ngati zemo ujikonda umwene palije malamulo ina yayakulu kupunda yaya."32Olemba wadakamba, "apuzisi mwakamba uzene Mulungu ndi mmoji ndi kuti palibe mwina kupunda iye. 33Kumkonda iye kwa mtima onche, ndi kwa mphavu zonche, ndi kumkonda kwa pafupi ngati umwene ndi vamate osati ngati nchembe ndi kupa viweto." 34Yesu yapo wadaona wayankha bwino wadamkambila, "iwe siulikutali ndi ufumu wa Mulungu," kuchokela paja palibe munthu ata mmoji wadayesa kumfuncha funcho lililonche Yesu.35Ndi Yesu wadayankha ndi wayaluza mkanisa wadakamba Bwa! Olemba akamba bwanji Kristo ndi mwana wa Daudi? 36Daudi mwene mwa Mzimu Oyera wadakamba Ambuye adakambila Ambuye wanga, kala kujanja langa la kwene m'baka nachite adani wako kukala panchi pa myendo yako. 37Daudi mwene wamtana Kristo Ambuye, bwa! Wakalancho bwanji mwana wake, gulu lonche limavechela mwa chisangalalo.38Mumayaluzo yake Yesu wadakamba, "jipenyeleni ndi olembaakumbila kuenda ndi nchalu za zitali ndi kulonjeledwa mmisika 39ndi kukala mmipando ya waakulu akulu mmasinagogi ndi mmasikukuu mmalo ya waakuluakulu. 40Akudya nyumba za ofedwa na achiamunao apempha mapemphelo ya yatali kuti wanthu aone wanthu anyiyawa saalandile chilango chachikulu."41Yesu wadali panchi pafupi ndi bokosi la anchembe mkati mwa hekalu wamapenya yao amachocha nchembe nkati mwa bokosi, wanthu ambili achuma adaika ndarama zambili. 42Ndipo mai mwina ofedwa ndi mmunake. Osauke wadaja ndi kutila senti ziwili mbokosimo.43Ndipo wadaatana opunzila wake ndi kula kuakambila zene ndikukambilani wamkazi ofedwa ndi mmunakeyu wachocha chachikulu kupunda onche atochocha m'bokosi la nchembeli. 44Ndande onche achocha kuchokana ndi kuchuluka kwa icho apata, nampho wamkazi ofedwa ndi mmunakeyu, kuchoka mosauka kwake wachocha ndarama iyo imafunika imtangatile mmoyo wake.''

Chapter 13

1Yesu yapo wadali niwaenda kuchokela muhekalu mmojhi wa opuzila wadamfuncha, "apuzisi penoyani myala ii yozizwicha ndi." 2Wadamkambila uona zinyumba izi zazikulu? Palibe ata mwala umojhi uwo siukhale pamwamba pa unjake uo siugwechedwa panchi."3Nae yapo wadakhala pamwamba pa phili la mizeituni kumbuyo kwa hekalu, Petro, Yakobo, Yohana na Andrea adamfuncha kwa chisisi, 4"tikambile vinthu ivi sivikhale chakhanji? Ndi chiyani dalili ya vinthu ivi kuchokela?"5Yesu wadayamba kwaakambila, "khalani maso kuti munthu waliyonche siwadakusokezani. 6Ambili siajhe kwa jhina langa naakamba, 'ine nde iye' ndi siwakoze ambili.7Yapo simuvele nkhondo, ndi minong'ono yankondo msadaopa, vinthu ivi ndi lazima vichokela nampho pothela pakali. 8Taifa siuinuke kinyume ndi taifa, ndi ufumu siuinuke ndi ufumu. Sipakhale ndi chintingiza pa malo yambili yambili, ndi njala. Ichi ni chiyambo cha utungu.9Khalani maso, siakupelekeni m'baka mmabwalo ndi sim'bulidwe pakati pa masinagogi. Simuimikidwe pachogolo pa otawala ndi ofumu kwa chifuko changa, ngati umboni kwao. 10Nampho mau la Mulungu, lazima huti likambilidwe kwa maiko yonche.11Yapo sakugwilicheni ndi, msadayambana kukhuza chijha icho simukambe. Mkati mwa nyengo imeneyo, simpachidwe chiyani chokamba, simukhala anyaimwe anyiyao simukambe. Nampho Mzimu Oyela. 12M'bale simshitaki m'bale kuphedwa, atate ndi mwana wao, wana siaime cha acha atate wao ndi kwachiticha kuphedwa. 13Simuipilidwe ndi kila munthu, kwa chifuko cha jhina langa. Nampho uyo siwalimbikile m'baka pothela, munthu uyu siwaomboledwe.14Yapo simuone choipicha cha kuwananga laima yapo yaposilifunika kuima (uyo wasoma ndi wajhiwe), nde ali mkati mwa Yuda athamangile mmaphili, 15nae uyo wali kumwamba kwa nyumba siwadachika panchi pa nyumba, kapena kutenga chalichonche chili pabwalo, 16ndi uyo wali kumunda siwadabwela kutenga chovala chake.17Nampho ole wao wachikazi ali ndi mimba ndi anyiyao ayamwicha pakati pa siku zimenezo! 18Pemphani kuti siidachokela nyengo ya mphepo. 19Kwani sipakhale ndi mavuto yakulu, yayo siyadawahi kuchokela. Kuyambila Mulungu yapo wadalikonja jhiko, mbaka saino, palibe wala siichokelancho. 20M'baka Ambuye yapo sazipunguze siku, palibe thupi ilo siliomboledwe, nampho kwa chifuko cha asankhulidwa anyiyao siwaasankhule, siapunguze namba za masiku.21Nyengo imeneyo ngati munthu waliyonche siwaakambile, penya, Kristo wali paho! Kapena, penya wali yapo. 22kwani akisto aunami ndi olosa aunami siachokele sachote ndi vozizwicha, ili kuti, akunyengeni, nampho ata. 23Khalani maso! Nathokukambilani yaya yonche kabla ya nyengo.24Nampho pambuyo pa mazunjo yaya ya siku izimenezo jhuwa silithilidwe mdima, mwezi siuchocha dangalila lake. 25Nthondwa sizigwe kuchokela kumwamba, ndi mphavu zili kumwamba sizitingizike. 26Ndeyapo samuone mwana wa Adamu niwajha mmitambo, kwa mphavu yaikulu kwa ufulu. 27Ndeyapo siwaatume angelo wake ndi kwaakusanya pamojhi ndi osankhidwa wake kuchoka nchonga zazikulu zinai za jhiko, kuchoka pothela pa jhiko mbaka pothela pa ntambo.28Kwa ntengo jiyaluzeni, ngati nthawi umo ikhozela kuchoka ndi kuika chisanga machamba yake, nde yapo simujhiwe kuti mwavuli pafupi. 29Nde umo ili, yapo simuone vinthu ivi nivichokela, jhiwani kuti wali pafupoi, ndi makomo.30Cha zene nikukambilani, uu ubazi siupita patali vinthu ivi sividachokele. 31Mtambo ndi jhiko sivipite, nampho mau yanga siyapita notho. 32Nampho kukhuza siku limenelo kapena nyengo, palibe uyo wajhiwa, ata angelo akumwamba, wala mwana, nampho Atate.33Khalani maso, penya, kwa chifuko simujhiwa ni nyengo yanji siyachokele. (Gwililila msari uu, mukhale openyelela, penyani ndi penyani ndi pemphani kwa chifuko, palibemo mnakala za kale). 34Ngati munthu wapita kuulendo; wadasiya nyumba yake, ndi kumuika mtumiki wake kukhala olamula wa nyumba, kila mmojhi ndi nchito yake. Ndi kumlamula openyelela kukhala maso.35Kwa chimwecho khalani maso! Ndande simujhiwa ni liti atate a nyumba yapo siabwele mnyumba, ikhozekhani ni ujhulo, usiku wa mamnane, nyengo nyengo tambala yaposiwalile, kapena umawa. 36Ngati siwajhe mchizulumukila, siwadakukomana wagona. 37Chijha nichikamba kwako, nichikamba kwa kila munthu: Kesheni''!

Chapter 14

1Idali siku pambuyo pasikuku ya Pasaka ndi mikate sidatilidwe chachu makuhani wakulu akulu ndi olemba adalikumfunafuna njila ya kumgwila Yesu kwa nchanje ndi khumpha. 2Pakuti adakamba, "osati nyengo ino yasikukuu wanthu siadaja kuchita fujho."3Nyengo Yesu yapowadali Bethania khukoma kwa Simoni, wamakhate, ndiyapo waelekea pameza, ukumkhazi mmojhi wadaja kwake wadali ndibotholo la marashi ya nardo yabwino yabwino ya mtengo oukulu kupunda wadaswa botolo ndikuipungula pamwamba pa munthu wake. 4Nampho kudali ndi baadhi yao anyiyao adakawia adakambilana achinawene adakamba, "ndi chiyani chifuko chakuthaika uku? 5Manukato yaya yadakhoza kugulichidwa kwa zaidi ya dinari miatatu, ndi kuphachidwa osauka," nao adamtutumila.6Nampho Yesu wadakamba, "msiyeni yokha, ndande yanji mumsumbua? Wachita nchintu cha bwino kwanga. 7Ntawi zonche osauka mlinao, nyengo yaliyonche yapomkhumbila mkhoza kuchita vabwino kwao. Nampho simukhala nane nyengo yonche. 8Wachita chija ichowachikhoza walipakha ntuphi langa mafuta kwa chifuko cha mazishi. 9Kwali ndikukambilani, kila pamalo injili intangazidwa jhiko lonche, chijha wadachichita wamkazi uyu sichizungulile kwa kumbukila kwake.10Pontela Yuda Iskariote, mmoji wa ayijha kumi ndi awili, adapita kwa waakuluakulu wa makuhani ili kuti apheze kumkadhi kwao. 11Nyengo wakuluakulu, wamakuhani yapoadavela chimwecho, adasekelela ndi adahaidi kumphacha ndalama, wadayamba kupenya nafasi ya kumkabidhi kwao.12Katika siku loyamba lamkate uosiudatilidwe chachu, nyengo adachocha mwana wa mbelele wa Pasaka, ophuzila wake adamkambila, "ufunathipile kuti tikaandae ili upate kudya mlo wa Pasaka." 13Wadatuma opunzila wake awili ndi kwaakambila, mapitani kuthauni, ndi wamuna uyo wabala mchuko siwaonane wamwe mchateni. 14Nyumba iyosiwalowe, mchateni ndi mkhambileni achinawene nyumba imeneyo aphuzisi wakamba chilikuti chumba cha alendo pamalo yaposindiye Pasaka ndi opuzila wanga?''15Siwangize chumba chakumwamba chachikulu cha mntengo ambacho chili tayari, chitani maandilizi kwa chifuko chanthu pajha. 16Opunzila adachoka adapita kutauni adapheza kila chinthu ngati umowadali wakambidwa ndi kuandaa chakudya cha Pasaka.17Nyengo yapoidali ujule wadajha ndi anyiwajha kumi ndi awili. 18Ndi yapoadali kuwandikila pameza ndikudya, Yesu wadakhamba, "kweli ndikukambilani, mmojhi kati yanu uyowakudya palimoji nane siwanisaliti." 19Wonche adandaula, ndi mmoji pambuyo pa mwina adamkambila, "uzene osati ine?"20Yesu wadayankha ndi kwaakambila, "nimmoji wa kumi ndi awili kati yanu, mmoji ambayo chipano wapojha ntonji katika bakuli pamoji nane. 21Pakuti mwana wa Adamu siwapate ngati mujha malembo yakhambila pamwamba pake nampho iole wake munthu yujha ambayo wapitila iye waadamu siwasalitidwe! Idakhakala bwino kupunda kwake ngati munthu yujha siwadakabodwa."22Ndi yapo adali nadya Yesu wadatenga mkate wadayankha, ndikuudula, wadaapacha wadakhamba, "tengani. Ili nde phuphi langa." 23Wadatenga chikombe, wadyamka, ndi kuwaphacha, ndi wonche adachimwela. 24Wadaakhambila, "uu ni mwanzi wanga waagano, mwanzi utaika kwa chifuko cha ambili. 25Kweli ndikukambilani, sinimwancho kupitila zao ili la mzabibu moaka siku lijha yapo sinimule mpya kupitila ufalme wa Mulungu."26Yapo adaphoimba nyimbo, adapita kubwalo kupitila phili la mizeituni. 27Yesu wadaakhambila, "anyiimwe mwaonche simkale patali kwa chifuko changa, pakuti yalembeledwa, sinditimbe owesa ndi mbelele sizisambalatike.'28Nampho pambuyo pakuhyuka kwanga, sinikuchogoleleni pachogolo panu Galilaya. 29Petro wadaakhambila, "atangati onche siakusie, ine sinikusia."30Yesu wadaakambila, "kweli nikukambilani usiku uno, kabla tambal siwadalile mara kawili, siikhale wanikana mara katatu." 31Nampho Petro wadakamba, "kumbe inilazimu kufa pamojhi nawe, sinikukana." Onche adachocha.32Adajha kueneo litanidwa Getsemane, ndi Yesu wadaakambila opuzila wake, "khalani yapa nyengo ndi phempha." 33Wadatenga Petro, Yakobo ndi Yohana palimoji nae, wadayamba kudandaula ndi kuhangaika sana. 34Wadakhambila, "nafsi yanga ili ndi Yohana palimoji naye, wadayamba kudandaula ndi kuhangaika sana."35Yesu wadapita pachogolo kidogo, wadagwa phanchi, wadaphempha, ngati idakhakozekana kuti ntawi ino. 36Nampho Yesu yapowadavela ambacho amakamba, adamkambila ochogoza masinagogi, Usidaopa, Amini pe."37Siwadamlamule walienche kuchogozana nae, ingakale Petro, Yakobo ndi Yohana m'bale wake Yakobo. ? 38Adaja kukomo kwa ochogoza wasinagogi nae wadapanya fujo, kulila kwambili ndi. '' 39Yapowadalowa mnyumba, adamkambila, ndande yanji mwadandaula ndi ndande yanji mulila? Mwana siwadafe ila wagona.40Adamseka, nampho iye, wadawachocha onche kubwalo adamtenga baba wa mwana ndi amani ndi anyiwaja adali pamoji naye, ndi adalowa mkati umowadali mwana. 41Wadatenga janja la mwana ndi adamkambila, "Talitha koum," ndi kukamba, "mwali wamng'ono ndikukambila, uuke. 42Ghafla mwana wadaukandi kuenda pakuti wadali ndi umli wa vyaka.''43Mara tu yapowadi wakali wamakamba, Yuda, mmoji wa anyiwaja kumbi ndi awili, wadafika ndikundi lalikulu kuchoka kwa waakuluakulu wa makuhani. 44Nyengo imeneyo msaliti wake wadali wadaapacha ishara, wadakamba yujha sinimbusu, ndeuy, umgwile ndi umpeke phanji pa oulonda. 45Nyengo Yuda yapowadafika, moja kwa moja wadaphita kwa Yesu ndi kukamba, "apuzisi!" ukabusu. 46Photela adamuika phaaaaaanji pa ulinzi ndi kumgwila.47Nampho mmoji kati yanu uyowadaima pafuphi nae wadasolomola upanga wake wadambula mtumiki wa kuhani wa mkulu ndi kumdula sikio. 48Yesu wadaakambila, "mwaja kunigwila kwa mau panga ndi vibonga ngati vibonga va anyang'anyi?" 49Nyengo kila siku nidali namwe ndi nimayaluza kuhekalu, simmanigwile, namphpo ili lachitika kuti malembo yakwanize. 50Na anyiwaja onche anyiyao adali ndi Yesu adamsiya ndi kuntawa.51Mnyamata mmoji wadamchata, uyowadavala shukatu wadali wadajibisa wadajivinikila kumzungulila, adamgwila nampho. 52Wadapokonyoka wadaisia shuka pajha wadatamanga maliseche.53Adamchogoza Yesu kwakuhani wamkulu pajha adakusanyika pamojhi nao makuhani waakulu akulu onche, azee, ndi waandishi. 54Petro nae wadamchata Yesu kwa patali, kuelekea kudua la kuhani wamkulu, wadakhala pamojhi ndi alinzi anyiwao pafuphi ndi moto ili kupheza mfundilo.55Nyengo imeneyo makuhani waakuluakulu onche ndi baraza lonche adali amafuna ushahidi pakati pa Yesu ili apate kumpha. Nampho siadapheze. 56Pakuti wantu ambili adapeleka ushuhuda wa mtila pakati pake, adakamba, nampho ata ushahidi wao siudalingane.57Baadhi yao adaimaima ndikupeleka ushahidi wa mtila pakati pake adakamba. 58Tidamvela niwakamba siniliwanange hekalu ili ilolakhonjedwa kwa manja, ndi mkati siku zitatu sinimange lina ilosilikonjedwa kwa manja. 59Nampho ata ushahidi wao siudalingane.60Kuhani wamkulu wadaima pakatikati pao ndi kumfunja Yesu, "bwa ulibe yankho? Wanthu anyiyawa ashuhudi chiyani pakati pako?" 61Nampho wadakala kimya ndi siwayankhe chalichonche, mara kuhani wamkulu adamfunchancho, "bwa iwe ni Kristo, mwana wa mbarikiwa?" 62Yesu wadakamba, "ine nde ine, ndi siumuona mwana wa Adamu wakhala janja la lwene la mphavu wakaja ndi mitambo yakumwamba."63Kuhani wamkulu wadang'amba chovala chake, ndikukamba, "bwa! tifuna mashahidi? 64Mwavela manyako, malamulo yanu ni yati?" Ndi wonche adamuhukumu ngati mmoji uyowafuka nyifa. 65Wina adayamba kumlavulila malovu ndi kumvinikila kumaso ndi kumbula ndi kumkambila, "tabiri," anchito adamtenga ndikumbula.66Ndi Petro yapowadali wakali phanchi kusel, mtumiki mmoji wa wachikazi wakkuhani wamkulu wadaja kwake. 67Adamuona Petro yapowadaima wamaotha moto ndi wadampenya kwakumsendelela pothela wadakamba, nawe udali Mnazareti, Yesu. 68Nampho wadakana, wadakamba, "sinijhiwa wasinielewa kuhusu chijha uchikamba!" Potela wadapita kubwalo kuseli (Zingatia; Mstari huu, "Na jogoo akawika" haumo kwenye nakala za kale).69Nampho mtumiki wamkazi pajha, wadamuona ndi wadayamba kwakambilancho wajha ambao adali adaimaima paja, "munthu uyu ni mmoji wao!" 70Nampho wadakanancho, pambuyo kidogo anyiwajha adaimaima pajha amamkambila Petro, "hakika iwe ni mmoji wao, kwachifuko iwe nawe ni Mgalilaya."71Nampho wadayamba kuijhika mwene phanchi pa laana ndi kulumbila, sindimjhi wa munthu uyu uyomumkhamba. 72Potela tambala wadalila mara ya kawili. Potela Petro wadakumbukila mau ambayo Yesu yayowamkambila, "kabla tambala siwadalile mara kawili, siunikane mara katatu," ndi wadagwa phanchi ndi kulila.

Chapter 15

1Umawa ni chisanga wakulu anchembe adapezane pamoji ni wazee ni otenga, nkhani ni gulu lonche la wazee. Ni kummanga Mpulumusi nikumpeleka kwa Pilato. Pilato wadamfuncha, "iwe nde Mfumu wa Wayahudi?" 2Wadamuyankha, "iwe wakamba chimwecho." 3Wakulu anchembe adakambilila yolakwa yambili wayachita Mpulumusi.4Pilato wadamfunchancho, "simuyankha chalichonche? Siuona umoakulalamikila kwa vinthu vambili?" 5Nampho Mpulumusi wadamuyankha Pilato, ni limenelo lidamdabulicha.6Kwa kawaida nthawi ya sikukuu, wammasulila omangidwa mmoji, omangidwa uyo amphempha. 7Kudali olakwa kundende, pamoji ni akupa kati ya olakwa atumikila yolakwa yao. Wadalipo munthu mmoji watanidwa Baraba. 8Gulu lidaja kwa Pilato, ni kumphempha wachita ngati umo wadachitila uko kumbuyo.9Pilato wadayankha ni kukamba, "mfuna nikumasulileni mfumu wa Wayahudi?" 10Pakuti wadajiwa ni kwandande ya nchanje wakulu anchembe adamgwila Mpulumusi ni kumpeleka kwa iye. 11Nampho wakulu anchembe adakwinjizila kuti gulu kubula pokoso kwa sauti kuti wamasulidwa Baraba badala yake.12Pilato wadayankha, ni kukamba, "nimchite chiyani Mfumu wa Wayahudi?" 13Adabula pokosoncho, "Mtese!"14Pilato wadauyankha, "wachita chinthu chanji choipa?" Nampho adapunda kubula pokoso, zambili zambili, "mtese." 15Pilato ni wafuna kwalizisha gulu, wadamasulila Baraba. Wadambula Mpulumusi viboko pambuyo wadamchocha dala amtese.16Asilikali adamchogoza mpaka mkati mwa seli (lija lili mkati mwa kambi) ni adakusanyika pamoji gulu la asilikali. 17Adamvela Mpulumusi, kanzu ya rangi ya zambarau ni adakonja taji ya minga adamvela. 18Adayamba kumzunja ni kukamba, "moni, mfumu wa Wayahudi."19Adambula kumutu kwa nchungwi ni kumlavulila malovu. Adabula magoti pachogolo pake kwa kumlemekeza. 20Ata akato mzalau, adamvula lija kanzu la langi ya zambalau ni kumvecha nchalu zake, ni kumchocha kubwalo kupita kumtesa. 21Adamlazimisha apita njila kumtangatila, uyo wa malowa kumbwani kuchoka kuvijijini. Watanidwa Simoni Mkirene (baba wake Iskanda ni Rufo); adamlazimisha kutenga mtanda wa Mpulumusi.22Asilikali adampeleka Mpulumusi pamalo patanidwa Goligotha (mate ya mau ili ni malo ya sanamu ya mutu). 23Adampacha mvinyo wachanganyidwa ni manemane, nampho wadamwe. 24Adamtesa ni adagawana nchalu yake, adayabulila chisankho kulamula chipande icho wapate kila msilikari.25Idali saa tatu umawa yapoadamsulibisha. 26Adaika pamwamba pake chibao chalembedwa dandaulo, "Mfumu wa Wayahudi." 27Adamtesa pamoji ni akuba awili, mmoji upande wake wa kwene ni mwina kumanjela kwake. 28(Kumbukila: Mzele uu, "ni malembo yadatimia yakamba," palijemo katika malembo ya kale).29Anyiyao amapita adamtukana, atingiza mitu yao akamba, Aha! Iwe ubomole nyumba ya mapemphelo ni kuimanga kwa siku zitatu, 30jilamiche umwene ni uchike pnchi kuchoka pamtanda!''31Kwa mtundu uuja wakulu anchembe adamzalau akambichana, pamoji ni otenga nkhani ni kukamba, "wadalamicha wina, nampho siwakoza kujilamicha mwene. 32Mpulumusi mfumu wa Israeli, chika panchi saino choka pamtanda, dala tikoze kupenyani kukukulupalila.33Idafika saa sita, mdima udaja pamaso pa jiko lonche mpaka saa tisa. 34Muda wa saa tisa, Mpulumusi wadabula pokoso kwa sauti yaikulu, "Eloi, Eloi, lama sabakhtani? Ikakala ni mate, "Mulungu wanga, Mulungu wanga, ndande chiani wanisia?" 35Baazi ya anyiyao adaima yapo adavela adakamba, "penya wamtana Eliya."36Munthu mmoji wadatamanga adajaza siki katikasponji ni kuiika pamwamba pa mtengo wa nchungwi wadampacha dala wamwe. Munthu mmoji wadakamba, "lindila tipenye ngati Eliya siwaja kumchicha panchi. 37Baadae Mpulumusi wadalila kwa sauti yaikulu ni wadafa. 38Pazia la nyumba ya mapemphelo lidagawanyika vipande viwili kuchoka kumwamb mpaka panchi.39Ofisa mmoji wadali waima wampenya Mpulumusi yapo wadaona wafe kwa ntundu uja, wadakamba, zene uyu munthu wadali Mwana wa Mlungu. 40Adalipo ni wachikazi anyiyao amampenya kwa patali kati yao wadalipo Mariamu (mama wake Yakobo mng'ono wa Yose), ni Salome. 41Muda wadali Kugalilaya adamchata ni kumtumikila. Niwachikazi wina ambili pia adapita nae mpaka Kuyerusalemu.42Yapo kudali ujul;o ni pakuti idali siku ya kujiandaa siku ya Sabato. 43Yusufu wa Arimathaya wadaja paja. Wadali ni mtenga wa baraza walemekezedwe munthu wakulupalila ufumu wa Mulungu. Kwa kujikulupalila wadapita kwa Pilato ni Afisa wadamfuncha ngati Mpulumusi wafa. 44Pilato wadadabwichidwa kuti Mpulumusi tayari wafa, wadamtana yuja Afisa wadamfuncha ngati Mpulumusi wafa.45Yapo wadapata uzene kwa Afisa kuti wafa, wadamruhusu Yusufu kulitenga tupi. 46Yusufu wadali wagula nchalu yoela. Wadamchicha kuchoka pamtanda, wadammanga kwa nchalu yoela nikumuika mkati mwa kaburi lakumbidwa katika pili ni wadaligunkhulicha mwala pakomo pakaburi. 47Mariamu Magdalena ni Mariamu mama wake Yose adaponya pamalo wakizidwa Mpulumusi.

Chapter 16

1Nyengo Sabata yapo idantha, Mariamu Madgdalena ndi Mariamu mama ake ndi Kaba, ndi Salome, adagula manukato ya bwino, ili ankaze kumuuncha kumpaka mafuta nthupi la Yesu kwa ajili ya kuzika. 2Umowa sana wa siku yoyamba ya juma, adapita kumakaburi nyengo jua lidaturuka.3Adakambana achinawene kwa achinawene, "yani siwavilinginche mwala, kwa ajili yathu ili tulowe mkaburi?" 4Nyengo yapo amapenya, adamwona munthu wantokuvilingincha mwala, uwo udali waukulu sana.5Adalowa muncha mkabuli ndi kumwona mnyamata wavala joho loela, wankala bendeka la kwene, ndi adadwaa. 6Wadankambila, "msidaopa. Mumfunafuna Yesu, wa Nazareti, uyo wadawambidwa. Wahyuka! Palipeba yapa. Penya pamalo yapo adamuika. 7Mapitani mkaakambile, opuzila wake ndi Petro kuti wachogolera kuelekea Kugalilaya kumeneka simumuone, ngati umowadambila."8Adachoka ndi kunthamanga kuchoka kumakaburi adatenthemela ndi adadwaa. Siadakambe chalichonche kwa munthu waliyonche ndande adaopa sana.9(Penya: Nakala za kale zilibe Marko 16:9-20) mapema kupitila siku yoyamba ya juma, baada yahyuka, wadaachokela kuti Mariamu Magdalena, ambaye kuchoka kwake wamchoncha mizimu saba. 10Wadachoka ndi kwaakambila anyiwancha anyiyawa adali pamoji naye, nyengo yapo wamadandaula ndi kuchocha misozi. 11Adavela kuti ndi wamoyo ndi waonekana naye. Nampho siadakulupalile.12(Penya: Nakala za kale zilibe MArko 16:9-20) baada ya yameneyo, wadajitokeza pakati kwa namna ya tafauti kwa wanthu wina awili, nyengo yapo amaenda kuchoka panchi. 13Adapita ndi kuwakambila opuzila wina anyiyao adabaki, nampho siadankulupalile.14(Penya: Nakala za kale zilibe Marko 16:9-20) Yesu pambuyo pake wadajitokeza kwaanyiwancha kumi ndi mmoji yapo adaegemea pameza ndi wadakalipila kwa kuta kunkulupalila kwao ndi kulimba kwa mitima yao. Ndande siadankulupalile anyiwancha adamuona baada ya kuhyuka kuchoka kwa akufa. 15Wadakambila mapitani jhiko lonche, ndi kukambilila mau la Mulungu kwa voumbidwa vonche. 16Waliyonche siwankulupalile ndi kubatizidwa siwaokoledwe. Ni yuncha siwankulupalila si wahukumidwe.17(Penya: Nakala za kale zilibe Marko 16:9-20) chiwalilo ichi sichigwilizane ndi wonche okulupalila. Kwa jina langa sianchonche mizimu. Siankambe kwa lugha ya mpya. 18Siagwile nchoka kwa mancha yao, ndi ata kumwachi nthu chalichonche cho tisha sichiwadhulu. Siaike mancha kwa odwala, nao siankale abwino."19Baada ya Ambuye kukamba nao, wadatengedwa kumwamba ndi wankala nchancha la kwene la Mulungu. 20Opuzila adachoka ndi kukambilila kila pamalo, nyengo Ambuye ndi achita nchito pamoji nao, ndi kulisibitisha mau kwa kudabwincha ndi chiwalilo chidanchatana nao.

Luke

Chapter 1

1Ambili adayesa kulongosola mbili ya vinthu ivo adavichita pakatikati pathu, ngati umoadatipachila ife, 2kuyamba po yamba ndi amboni amaso ndi atumiki authenga. 3Kwaicho ine nane, pokhapenya bwino, chiyambo cha nkhani izi zonche chiyambile nemayambo ndaona bwino kwaine kukulembela bwino olemekheleka Theofilo. 4Kuti ukhote kujhiwa uzene waizo wayaluzidwa.5Nyengo ijya ya mfumu Herode, wa ku Yudea, wadalipo wanchembe mwina wamatanidwa Zakaria wa fuko la Abiya. Mkazi wake wa machokhela fuko la Haruni jhina lake wa matanidwa Elizabeti. 6Wonche adali olungama pamaso pa Mlungu, amaenda mokuluphilika mmalamulo yonche. 7Nampho adalijhe mwana, ndande Elizabethi wadali munthu osabale, ndinyengo ino wonche okhota kupunda.8Idaoneka kuti Zakaria olalikila, wadaendekele ndi nchito yake ya Uchembe panyengo yakhe. 9Po chata dongosolo la kusankha wanchembe yuthi wadasankhidwa kuchitidwila chisankho kulowa mnyumba ya Mulungu ndi kwaishi wakada fukiza lubani. 10Laelu lonche la wanthu limaphemphera kubhwalo yapho amafukiza lubani.1113Chiphano mbelo wa ambuye wadamuo nekhela ndi kuima jhanja la kwene mkati mwa guwa pakufukiza. 12Zakaria wadaofyeka yapho wadamuona; mantha yadamgwela. Nampho mngelo wadamkhambila, "Usaopa Zakaria, ndande maphemphero yako yavekha. Mkazako Elizabeth siwakubalila mwana. Ndi jhina lake siumthane Yohana.14Siukhale okhondwa ndi kusangalala ambili sakhukondwele kubadwa kwake. 15Pakuti siwakhale wamkulu pamaso pa ambuye, siwamwa vinyo kapina cha khumwa chokalipa, ndisiwakhali wajhazidwa mzimu oyera chiyambile mmimba mwaamake.16Ndi wanthu ambili aku Israeli sanibwelele Mbuye Mlungu wao. 17Siwapite pachogolo pamaso pa ambuye mkati mwa mzimu ndi pamvu za Eliya. Siwachite chimwechi kubweza mitima ya atate kwa wana, kuti opande ulemu akha ndi njelu ya olungama.''18Zakaria wadamkambila mgelo, "Sindikhoze bwanji kujhiwa izi? Chifukwa ine nadakotha ndi mkazi wanga viaka vake vakhala vambili kupunda." 19Mngelo wadayankha ndi kumkhambila, ine nde Gabrieli, ndiima pamaso pa Mulungu. Ndidatumidwa kukukambila, kukupelekela nkhani iyi ya bwino. 20Ndi ona, siuphenya, siukhale chete, siukhoza kukhamba mbakaa sikhu lijha izi yapho sizichokhele, ndande udalepela kukhulupalila mauyanga yayo siyakwanile msanga."21Wanthu amamlindilila Zakaria. Amazizwa kuti wamatumikila nyengo ya mbili mnyumba ya Mulungu. 22Nampho yapo wadatuluka kubwalo, siwadakhoze kukamba nao, adajhiwa kuti mnyumba ya Mulungu mujha waona chinthu mmasophenya. Wadaendekhela kulangiza chizindikilo ndi kukhala chete. 23Masikhu ya utumiki wake mnyumba ya Mulungu yapo yadata idaoneka wadacho kha kubhwela kukhomo lake.24Pambuyo pake Zakaria kubwela kukhomo lake kuchokela mnyumba ya Mulungu, mkazake wadali ndi pathupi. Naye ncho siwadachoke pakhomo lake panthawi ya miezi isano. 25"Izi nde izo ambuye andichitila ine yapo adandipenya pa chifundo chao pondichochela manyazi pakati pa wanthu."2628Chiphano, Elizabethi wali ndi pathupi pa miyezi isano ndi umojhi, Mlungu wada mkambila mngelo Gabrieli kupita kumujhi wa Galilaya utanidwa Nazareti, 27Wadamtuma kwa wamkazi wadali osamjhiwe wa mmuna wadachumbidwa ndiwammuna iye jhina lake lidali Yusufu. Iye wadali wafuko la Daudi, ndi jhina osajhiwa wa mmuna uyu lidali Mariamu. Adajha kwaiye ndikunena, "Moni, iwe walandila mtendere! Wakondwecha ambuye." 29Nampho mau ya mbelo yadamjujumucha ndisiwadajhiwe ndande chiyani mngelo wadamlonjela moni yodabwicha iye.30Mngelo wadamkhambila, "Usaopha, Mariamu, chifukwa Mlungu wakuonekhela. 31Ndi onani, siume mimba ndisiubale mwana . Ndi siumtane jhina lake 'Yesu'. 32Siwakhale wamkhulu ndi siwatanidwe mwana wa uyo walikumwamba kupunda ambuye Mlungu sampache mpando wa chifumu wa Daudi tata wake. 33Siwalamulile fuko la Yakobo muyaya ndi ufumu wake siukhale muyaya.34Mariamu wadamkhambila mngelo, izi sizioneke pa mtundu uti, pakuti sindidagonepo ndi wammuna waliyenche? 35Mngelo wadayankha ndikumkhambila, siukhuchikile mzimu oyera, ndi mphamvuya uyo walikumwamba kupunda sikujele iwe kwaicho, oyera uyo siwabadwe siwatanidwe mwana wa Mlungu.36Ndi ona, mbale wako Elizabeti wali ndipathupi pa mwana wake wakuukhota. Uno ndi miyezi isano ndi umojhi kwaiye uyo wamatanidwa sabala. 37Pakuti palijhe icho sichikhozekana kwa Mlungu." 38Mariamu wadakamba, "Onani ine ndi wanchito wa mkazi wa ambuye. Siya ikhale chimwecho kwaine kufanana ndi uthenga wako." Ndipo mngelo wadamsia.39Nde pamasikulu yajha Mariamu wadachokha ndi msanga wadapita kujhilola maphili maphili, mmujhi wa jhiko la Yudea. 40Wadapita mnyumba mwa Zakaria mjhiko la maphili ndikumlonjela Elizabeti. 41Chipano, idachokhela kuti Elizabeti yapo wadavela moni ya Mariamu, mwana mmimba mwake wadalumpha, ndi mzimu oyera udamchikhila Elizabeti.42Wadakweza mau yake ndi kukhamba kwamphamvu, wadalisidwa kupunda iwe kuposa wachikazi wonche, ndimwana wali mmimba mwako wadalisidwa. 43Ndiyakhala bwanji kwaine kuti, mwana waambuye wangu wadafunika wajhe kwa ine? 44Penya pakuti yapo idaveka mmakutu mwanga moni yanu, mwana mmimba mwanga wadalumpha mwachisangalala. 45Ndi wadilisidwa wamkazi yujha wada khulupalila kuchokela chikwanilo cha izo adakambidwa kuchokea kwa ambuye.''46Mariamu wadakamba, mtima wanga ukutamanda Ambuye, 47ndi mzimu wanga wakondwelela Mlungu mphulumusi wanga.48Pakuti walowelela lamidwe la panchi la mtumike wake wamkazi. Ona, chiyambile chipano vibadwa vonche sivinditane odalisidwa. 49Pakuti iye walindi phamvu wachita zazikulu, ndi jhina lake ndi loyera.50Chifundo chake chikhale kuyambila chibadwa mbakana chibadwa waanyiwajha amlemekeza iye. 51Pajanja lake walangiza mphamvu, wabala licha anyiwajha amitima wonyada.52Wachicha panchi mafumu amphamvu pamipando yao ya chifumu, ndi kwa kweza wanthuwamba. 53Anjala wadaakhuticha vinthu vabwino, nampho olemela wadaatophole manja ya chajhe.54Wamtandiza Israeli wanchito wake, po kumbukila chifundo chake 55(ngati umo wadakambila kwa acha atate wathu) kwa Abrahamu ndi vibadwa vake muyaya."56Mariamu wadakhala ndi Elizabeti ngati mwa miyezi itatu nde yapo wadabwela kukhomo lake. 57Nthawi ya Elizabeti kujimasula mwana yapo idakwana wake ndi wadaji masula mwana wa mmuna. 58Aphafupi ndi mabale wake yapo adavela kuti ambuye amchitila chifundo chachi khulu, adakonda pamojhi ndi iye.59Pa masiku asano ndi ya tatu adajha kumuumbala mwana. Adafunikha kumphacha jhina la atate wake Zakaria," 60nampho amake adayankha ndi kukamba, iyayi, siwatanidwe Yohana." 61Adamkambila, hata mmojhi mwamabale wako watanidwa kwa jhina ili."62Adamchitila chizindikilo tate wake kuti iye wadafuna jhina watanidwe yani. 63Tate wake wadafuna cholembela kuti walembe, ndi wadalemba, jhina lake ndi Yohana.64Mwazizi pakamwa pake padamasuka ndi kuyamba ndikutamanda Mlungu. 65Amakhala pafupi na anyaio yadaagwila mantha, mbili iyi idaenela jhiko lonche la maphili ya ku Yudea. 66Ndiwonche yao adavela adayaika mmitima mwao, ndiadakamba mwana uyu wa mtundu wanji?" Ndande juanja la ambuye lidali pamojhi ndiiye.67Atate wake Zakaria adajhazidwa ndi mzimu oyera ndi kuchocha ulosi, ndi kukhamba, 68"Atamandike ambuye, Mlungu waku Israeli, chifukwa watandila kuombola wanthu wake.69Watiuchila uomboli mkati mwanyumba ya mtumiki wake Daudi, kuchokela kufuko la mtumiki wake Daudi, 70ngati umowadakambila kupitila mlosi wake uyo wadalipo kale. 71Tiomboledwe nda adani watu ndi mmanja mwaonchi yao adana ndi ife.72Siwachite chimwechi kulangiza chifundo kwa achambuyatu, ndikukumbukira chipangano chake choyera, 73lumbilo ilo wadakamba kwa atate wathu Abrahamu. 74Wadalumbila kuti kumtumikila iye popande mantha, pambuyo po omboledwa kuchokha mmanja mwa adani wathu. 75Kuti tikhale oyera mtima ndi olungama pamaso pake masiku yathu yonche.76Etu, ndiiwe mwana, siutanidwe mlosi wa kumwamba kupinda, pakuti siupite pachogolo pa ambuye kuti wamkonjele njila, kwakonjua wanthu ndande ya kujua kwake, 77kuwajhiwicha wanthu wake kuti, saombo ledwe kwa njhila yolekheledwa machimo yao.78Silichokele ili ndande ya lisungula Mlungu wathu, ndande jhua kuchokela kumwamba siliti jhele, 79kwaawalila anyiao akhala kumdima siwachite chimweche kuichogoza miyendo yathu mnjila ya mtendele."80Chipano yujha mwana wadakhula ndi kukhala ndi mphamru za mumtima ndi wadakhala mtengo mbakana yapho wadaoneka kwa Aisraeli.

Chapter 2

1Cho pano panyengo zimenezo, idachokela kuti Kaisari Agusto wadachocho malangizo wamakambila kuti tenge lani chiwelengelo cha wandu onje yao akala panji. 2Iyi idati ndi chiwelengelo cho yambachida chitika nyengo Krenio wadali wakulu wa Siria. 3Ndipo kila mmoji wadapita kumjini kwake kulembecha chiwelengelo.4Nae Yusufu wadachoka pa muji wa Nazareti kumene ku Galilaya ndiwada wadanyamuka ku Yudea pamuji wa Bethlehemu, ufuwika angati muji wa Daudi, pandande wadachokela pa nkolo la Daudi. 5Wadapita kumeneko kujilembecha pamoji ndi Mariamu, uyo wadali wakwata ndi wadali ndiwa embekezeta mwana.6Chopano idachokela kunti, ali kuja ndawi yake yojimasula mwana ufifika. 7Wadajimasula mwana wamuna, mbadwa wake oyamba, wada vilingila njala mtupi kumchinga ndi mbepo mwana. Wadamwika mkola lonjechela vinyama, pandande padalibe mpata mnyumba zalendo.8Pamulo ilo, adali owesa yayo amakala owesa yaomakulu mminda vidali vikundi va mbelele zao usiku. 9Chizulumikilo, angelo wa mbuye wadafela, ndi m'bavu za mbuye zidang'ala kwazungulila, ndi adali ndi manda kupunda.10Ndiposo angelo wadakambila, "Msidaopa, pandande ndikupelekelani nkuni yabwino iyo sikupelekeleni chisangalalo chachikulu kwa wandu onje. 11Lele otuombola wabadwa ndande yaife bwani ya Daudi! Iye nde Kristo Ambuye! 12Yaya ndemau yayo simuningidwe, simupeze mwana wanangidwa njalundi wang'ona mkola lo jechela vinyama.''13Pachizulumukilo kudali ndi abolisi ambili kumwamba adagwilana ndiangelo adamuyamika Mulungu, 14ufulu wa Mulungu ulikumwamba kupunda nditendele ukale ukale panji ndi onfe ya akondedwa nao."15Idali kuatnti angero yapowadali kuchoka kupita kumwamba owesa adakambilana iwondi iwo, tieni chopano kuja ku Bethlehemu, ntikaone ichi chindu icho chakochela, icho ambuye atijiwicha." 16Adayanguka kuja, adampeza Mariamu ndi Yusufu, adamuona mwana wangona mkola lojechela vinyama."17Ndiyapo adaona ichi wadajiwicha wantu chija adali kukambili dwa kuhusu mwana. 18Onje yao adavela ngani li adadabwi chidwa ndi icho chida kambidwa ndi owesa. 19Nambo Mariamu wadaendekela kuganiza kuhusu yonje wadali kuyavela wadayaika mutima mwake 20Owesa adabwela ndi nkunkuza ndi kumuyamika Mulungu pandande ichi chindu icho adati kuvela ndi kupenya, ngati monga idakambidwa kwanyiiwo.21Yapo idafika siku ya nane ndi idali nyengo yakumdula mwana, adamtana jina Yesu, fina ilowato ningidwa ndi yuja ungelo pambuyo pamimba sichi mmimba.22Zanyiiwa izo zimafunika ndizojikonja zidapita, vufanana, ndilamulo ya Musa, Yusufu ndi Mariamu adampeleka mnyumba kuja ku Yerusalemu kumwika pachogolo pa Mbuye. 23Ngati omoidalembedwa palamulo lambuye siwatanidwe uyo wachochedwa mbaso kwa Mbuye." 24Anyiiwa chocho adaja kuchocha mbaso kulingana ndi chija chikambidwa pa malamulo ya Mbuye, "Jozi la njiwa au wana awili ya ngunda."25Penyani kudali ndi mundu pa Yeusalemu ndipo jina lake wamatumidwa Simeoni. Mundu mmeneyo wadali ndi maenelo ndi okulupilila Mulungu iye wadidiwalila ndande ya mundu wa kusihi Israeli ndi mtima wa ufulu udali pamwamba pake. 26Idali yarito kuta kumasulidwa kupitila mtima oyela kuti iye wadakafa pambuyo pomumwo na Kristo wa Mbuye.27Siku limoji wadaja nyumba ya ndiwachongo zedwa ndi mzimu oyela. Ndipo makolo adampeleka mwana, Yesu, kuchitila yajayadakambidwa palamulo, 28ndi poso Simeoni wadalandila mmaja mwake, ndi kumuyamika Mulungu ndi kukamba, 29"Chopano vomeleza mtumiki wako wapite pamtendele Ambuye, kufanana ndi maulanu.30Pakuti maso yanga yapenya ufulu wanu, 31uyo waonekana pamaso pawandu onje, 32iye ndi nyali pandande yomasulidwa pajiko ndi.''33Atate ndi amai amwana adadabwichichwa ndimau yadakambidwa pamwamba pake. 34Nde Simeoni wadaika manja ndikukkamba kwa Mariamu amayiwake, "Vechela lovechela mwana uyu si wakale ndande yosowa ndikupulumusidwa kwandu ambili pakati pa Israeli ndi chijho chawanda ambili saikane. 35Ndipo ndichikwanje icho sichitose mtima wako umwene, ndiposlo mitima ya wandu ambili yadawanangika."36Mtumiki wakazi uyo wama tanidwa ananaye wadalipo mnyumba. Iye wadali mwali wa Fanueli kuchoka pakolo la Asheri. Wadali ndi vyakavambili kupunda. Nae wadakala ndi mamuna wake vyaka saba badala yo kwatilana, 37ndiposo wadali osakwatiwa pavyakathemani ni ndivyaka vinai nayo si wadai kuchoka mnyumba yambuye ndi wapembela Mulungu ndikumanga kujandi kupemba, usiku ndi usana. 38Ndi pandawi imeneyo wadabwela paja adali ndi kumuyamika Ambuye. Wadakamba ngani ya mwana kwa kila mundu walalindiwaalinda kuelesedwa kwa Yerusalemu.39Yapo adamaliza kulachinda ifo chidabidi kuchita kulingana ndi malamulo ya Mbuye, adabwela ku Galilaya, kumjini kwao, ku Nazareti. 40Mwana wadali, ndi wadali ndimba, uwamaongezeka pakuti pazelu, ndi ufulu wa Mulungu udali pamwamba pake.41Makolo yake kila chaka amapita ku Yerusalemu ndande yachisangalalo cha Pasaka. 42Yapo wadali ndivyaka kumi ndi viwili adapitanjo pandawi yokwana ngati chilangizo pandande ya chisangalalo. 43Pamboyo pokala vyaka pandande ya chisangalalo, adayamba kubwela kukomo. Nambo mamuna Yesu wadakali kumbuyo kuja ku Yerusalemu ndi makolo wake samajiwe ichi. 44Amakhani kuti walipo mukundi ilo adali ama chokanalo, chocho adanyamuka ndawi ya siku. Ndiposo adayamba kumfuna mmalo mwacha abale ndimabwwenjilao.45Yapo adalepela kumpeza, adabwela ku Yerusalemu ndiposo adayamba kumfuna kumeko. 46Chida chitika kuti panyengo ya siku zi tatu, adampata mnyumba wali wakla pakati pa apuzisi, ndi wavechela ndikwa fusa mafuso. 47Onje yao adamvechela amadabwandi zelu zake ndi mayango yake.48Yapo adampeza adadabwa. Amai wake wadamkambila, "Mwana wanga ndande yanji watichitaichi? Vechela atate wako ndi ine timakufuna kujiopye za kupunda." 49Wadakambila, "Ndande yanji mmanifuna? Simudajiwe kuti inibidi ni kale mnyumba ya atate wanga? 50Nambo yadave icho wamalinga pamau yameneyo.51Ndiposa wadanyamuka nayo nawo mbaka kukomo ku Nazareti ndi wadali overa. Kwao amayo wake adaika mau yake mutima mwao. 52Nambo Yesu wada endekela kukulandizelu ndi vyaka, ndi wadaendekela kukondedwa ndi Mulungu ndi wandu.

Chapter 3

1Chapano pakasi pa chaka cha kumi ndi zisano paulamulilo wa Kaisari Tiberia, nfawi Pontio Pilato wadali wa mkuru wa malo ya Uyahudi, Herode wadali wa mkuru wa mkoa wa Galilaya, ndi Filipo mbale wake waderi wa mkuru wa mkoa wa Iturea ndi Trakoniti ndi Lisania wa dari wa mkuru wa mkoa wa Abilene, 2ndi ntawi ya upadi wa mkuru wa Anasi ndi Kayafa, mau la Mulungu lidemyera Yohana mwana wa Zakaria, pamdengadenga.3Wadaenda pakati kati pa mkoa woche kuzungulila mchinje Yordani, ndi wakambilila kurapa chifuko cha kulekelela machiri dwe yoipa.4Ngasi mmene ida lambedwela mkati mwachikalakalacha mau ya Isaya olofa, mau ya muntu wali mtengo ikonjeni njira ya Murungu, yakonjeni moendela mwake mwa mukole mwabwino.5Mgombe mumonche si mubwezedwele bwino mepiri yali yonche udipiri siyakare bwino, njira ziwene sizide kalebwinu sizikale zabwino ndi njira zedangu kwalidwa sizikale bwino. 6Wantu wonche siapeze uperumuchi wa Murungu."7Mmwemo Yohana wada akambila wantu ambili adalipo kunjera nanancho abatizidwe ndiiye anyiimwe mbadwa za njoka mindifumo yani wada kuofyezani kuitawa mpwayi ikuja?8Mbare vipacho vichetane ndi kulapa ndi si mdayamba kukamba mkati mwake, "Tiliweye Ibrahimu imeneyo wali tata watu chifukwa chake ndikukambihani Mulungu wako zakumnyakulila Ibrahimu wana kuchokela mmial iyi.9Tayari ukwanga yaikidwa mmizo ya mtango kwa mmwemo mtengo ulionche wapande vipacho valowiwo siudulidwe ndi kufaicha kuwofo.10Pambuyo pake wantu ade mfuecha ndi akamba, "Chapano tifunika jichite bwanji?" 11Wade ayauka ndikwa akambisa, 'Ngati muufu wali ndi kanzu ziwili ifunike nachoche imosi kwa mujake mmene walije letu ndivyo wali ndi chakudya wachite chimwecho mwecho."12Pambuyo pake watu ochepa amadulicha msouko adaja kubatiza ndiada mfuncha mwalimu lichite bwanji? 13Side sonkanicha ndalama zembili kupanda chimenecho mfunidwa kulonganicha."14Aliochepa azankondo adamfuncha ndiife bwanji tifunike tichite bwanji wade akambila msada feapa ndelema kwa mwutu waliyenche mwanjira ya mpanu ndu simda mfa nizile mwafu waliyenche mwanjira ya unaani mkurupalile mikokolo yanu."15Chapano chifuko waufu adali ni kumbilo ya kulidiila Kristo uyusiwabwele aliyenche wadili ndiganizo momfire mwake kupitila Yohana ngati iye ndiye Kristo. 16Yohana wade yauka kwa kambala onche, "Ine ndikubasizauni anyuimwe ndi maji nampo waapo mmoji wali ndumparu kupunde fwe ndisindi funika atakumaswa malusu ya vilaso vake siwa kubapizeni anyume kwa mzino Oyera ndi kwa moto.17Lichelo lake lili mmaja mwake nampo dala kuyelecha bwino mato yake ya kupetela ngano ndi kuisika pamoji ngano mnkokwe mwake nampo siwanange kupete ndimoto uweneo wasafiudwa.18Kwa kuopyeza yena yambili wada kambilila nkeni zabwilo kwawantu wonche. 19Yohana wada mkalipira kuponda Herode wamkuru wa mkoa kwa kuukwatira Herodia, wamkezi wa mbale wake ndikeyaioa yene yonche yawewe Herode wadeya chita. 20Nampo pambuyo pake wadechita choyoopa yoipa kupundi chicha wade mmanga Yohana mchisolokosi.21Pambuyo pake pachokele kuti udawi zonche wannfuyapo anabasizidwa ndi Yohana ne yenche Yesu wadebasizidwa pawene wapempele mafumbo idamasuka. 22Mzimu woyela wadachika kwa chifwani fani cha chifupofupo ngati nkunde ufwani yomweyo mane lifafika kuchikele kwa mwamba ndi ikaamba iwende mwana wanga okondedwa ndikondedwe kupande ndidwe."23Chapano Yesu mwene wake yapo wadayamba kuyaruza hadeli ndi viakangasi thelathini. Wadali nde mwana (ngasi mmene idaganizilidwa) wa Yusufu, mwana wa Eli, 24mwana wa Mathati, mwana wa Lawi, mwana wa Melki, mwana wa Yana, mwana wa Yusufu,25mwana wa Matathia, mwana wa Amosi, mwana wa Nahumu, mwana wa Esli, mwana wa Nagai, 26mwana wa Maati, mwana wa Matathia, mwana wa Semeini, mwana wa Yusufu, mwana wa Yuda,27mwana wa Yoanani, mwana wa Resa, mwana wa Zerubabeli, mwana wa Shealtieli, mwana wa Neri, 28mwana wa Melki, mwana wa Adi, mwana wa Kosamu, mwana wa Elmadamu, mwana wa Eri, 29mwana wa Yoshua, mwana wa Eliezeri,, mwana wa Yorimu, mwana wa Matathi, mwana wa Lawi,30mwana wa Simeoni, mwana wa Yuda, mwana wa Yusufu, mwana wa Yonamu, mwana wa Eliyakimu, 31mwana wa Melea, mwana wa Mena, mwana wa Matatha, mwana wa Nathani, mwana wa Daudi, 32mwana wa Yese, mwana wa Obedi, mwana wa Boazi, mwana wa Salmoni, mwana wa Nashoni,33mwana wa Abinadabu, mwana wa Aramu, mwana wa Hesroni,, mwana wa Peresi, mwana wa Yuda, 34mwana wa Yakobo, mwana wa Isaka, mwana wa Ibrahimu, mwana wa Tera, mwana wa Nahori, 35mwana wa Seruig, mwana wa Ragau, mwana wa Pelegi, mwana wa Eberi, mwana wa Sala,36mwana wa Kenani, mwana wa Arfaksadi, mwana wa Shemu, mwana wa Nuhu, mwana wa Lameki, 37mwana wa Methusela, mwana wa Henoko, mwana wa Yaredi, mwana Mahalalei, mwana wa Kenani, 38mwana wa Enoshi, mwana wa Sethi, mwana wa Adamu, mwana wa Mungu.

Chapter 4

1Ndipo Yesu yapo wadajhala mzimu Oyela, wadabwela kuchokela kumchinje Yordani, ndi kuchogoze dwa ndi mzimu kupululu 2kwa masiku arobaini nai kumeneko wadayesedwa ndi satana. Nyengo jineneyo siwadedye chesichondhe, ndi potela pauyengo imeneyo wadajivicha njala.3Satana adamkambila, "Ngati iwe ni mwana wa Mulungu, ulamulile mwala uwukuti mkate." 4Yesu wadamuyankha, "Yalembedwa; mundhu siwalama kwa mkate booka."57Ndipo Satana adamchogoza kumwamba mwotela mwa pili, ndi kumlangiza fumu zonche za jhiko kwa ntawi ya ifupi. 6Satana adamkambila, "Sindikupache malamulo ya kuchogoza fumu izi zonche pamojhi ndi vokaduilicha vake. Ndikoza kuchita vimenevo kwa chifuko vonche napachidwa ine ndi viimilile, ndi nikoza kumpacha waliyeuche sinifune kumpacha. Kwa icho, ngati siunikwatamile ndi kunilambila, vindhu ivi vonche sivivale vako."8Nampho Yesu wadayankha nai kumkambila, "Yalembedwa, "Nditu umlambile Ambuye Mulungu wako, ndi nditu umgwilile lye yokape."9Pambuyo Satana adamchogoza Yesu mpakana ku Yerusalemu ndi kumuyika pamalo pa pamwamba kupitilila pa nyumba ya Mulungu ndi kumkambila, "Ngati iwe ndi mwana wa Mulungu, jhitaye panchi kuchokela pano. 10Kwa chifuko yalembedwa, siwakutumizileni angelo wake wakusungeni ndi kukuimilila, 11ndi siwakukweze kumwamba mmanja mwao ili kuti usadapwetekecha myendo yako pamwamba pa mwala."12Yesu wadayankha wadakamba, "Yanenedwa, "Usadamuesa Ambuye Mulungu wako." 13Satana yapowadamalize kumuyesa Yesu, wadapita ndi kumsiya mpakana nyengo yena.14Ndipo Yesu wadabwela ku Galilaya kwa mphavu za mzimu, ndi nkhani jmamkuza lye zidawanda ndi kuvekela mikoa ya yowandikila yonche. 15Wadayaluza pa masinagogi yawo, ndi kila mmojhi wadamtogoza.16Siku limojhi wadapita ku Nazareti, mujhi uwo wadaleledwa ndi kukulila. Ngati uwo idari mtundu wake wadalowa musinagogi siku ya sabato, ndi wadayima kusoma malembo. 17Wadapachidwa chikalakala cha olosa Isaya, mmwemo, wadamasula chikalakala ndi kufunafuna pamelo palembedwa,18"Mzimu wa Mbuye uli kumwamba kwanga, chifuko wadanitila mafuta kulalika mchani za bwino kwa osauka. Wanituma kutangasila ufulu kwayawo omangidwa, ndi kuwachita yawo osapeuya akoze kupenyancho. Kwaika ufulu auyiwajha anyikizilidwa, 19Kutangaza chaka icho Ambuye siwalangize ubwino wake."20Ndipo wadamasula gombo, wadambwezela ochogoza wa sinagogi, ndi kukala panchi. Maso ya wandhu wonche adali pa sinagogi yadampenya iye. 21Wadayamba kucheza nawo kunena, "Lelo lembo ili lakwani chifidwa masikio mwanu." 22Kila mmojhi pajha wadachitaomboni chijhe wadanena Yesu, ndi wanyinyi mwanyilwo adadabwichidwa ndi mau ya ulemu yayo yamachoka mkamwa mwake. Amanena, "Uyu ndi mnyamatape wa Yusufu, osati chimwecho?"23Yesu adakambila, "Zene simnene chindapi ichi kwaine, "Sing'anga, jilamiche wa mwene. Chalichonche tachivela niuchita ku Kapernaumu, chichite panoncho pachijhijhi pako." 24Naphoncho adanena, "Zene nikukambilani anyiimwe, palibe mlosi wavomeleka kujhiko lake."25Nampho nikukambilani anyiimwe uzene kuti adalipo ndi ofedwa ndi wachimuna ambili ku Israeli panyengo ya Eliya, nyengo kumwamba kudamangidwa kusadakala ndi vula kwa vyaka miatatu ndi nusu, nyengo yapokudali ndi njala yaikulu pa jhiko lonche. 26Nampho Eliya siwadatumidwe kwa waliyenche mmojhi wa anyiiwo, nampho ofedwa ndi wamuna mmojhi yeka, uyo wamakala kusarepta pafupi ndi mujhi wa Sidoni. 27Pamwepoje, adalipo ndi amakate ambili Israeli pa uyengo ya Elisha olosa, nampho palibe atammojhi wawo wadalamichidwa ikapanda Naamani mundhu waku Siria.28Wandhu wonche mkati mwa sinagogi adasi ndi mphwayi yapoadavela yameneyo yonche. 29Adaima ndi kumbwanyizila kubwalo kwa mujhi, ndi kumchogoza mpakana mubhepete mwa pili mwa mujhi pamene mujhi udamangidwa pamwamba pake, kuti akoze kumtaya panchi. 30Nampho wadapita mtendele pakatikati pawo ndi kuendekela ulendo.3132Ndipo wadachikilila ku Kapernaumu, pa mujhi wa Galilaya. Sabato imojhi wadali mkuyaluza wandhu mkati mwa sinagogi. Adazizwichidwa ndi mayaluzo yake, kwa chifuko wadaluza kwa malamulo.3334Chipano siku limelo mkati mwa sinagogi, kuzali ndi mundhu wadali ndi mzimu chiura choipa ndi kulila kwa kuvekela kwa pamwamba, "Tili nichiyani ndiiwe, Yesu waku Nazareti? Nijhiwa ifwe ni yani! Iwe ni woyela wa Mulungu!"35Yesu wadamkalipila chiuta kunena, "Kachete ndi mchoke mundhu uyu!" Chiuta yujha yapowadamponya mundhu yujha panchi pakatikati pawo, wadamchoka yujha mundhu popande kumchitila vopweteka valivonche. 36Wandhu wonche adadabwa, ndi kuendekela kukambilila mchani imeneyo kila mmojhi ndi mujake. Kunena, "Ndi mau ya mtundu wanji yaya?" Walamulila mizimu oyipa kwa malamulo ndi mmphavu ndi kuchoka. 37Kwa mmwemo, nkhani pa mwamba pa Yesu zidawanda kila amalo pazungululila mkoa umeneo.38Ndipo Yesu wadachoka pa mujhi umeneo ndi kulowa pa nyumba ya Simoni. Chipano apongozi wake ndi Simoni adali odwala malungo yokalipa, nde ada mphembha pa malo pa iye. 39Ndipo, Yesu adamsendelela, kuyakatipila malungo jajha ndi kumsilila. Mwachizulu mukilila wadaima ndi kuyamba utumiki.40Jhuwa yapo limabila, wandhu adampelekela Yesu kila mmojhi wadali odwala wa vilombo va kila mtundu. Wadayika manja yake pamwamba pa kila odwala ndi kwalamicha wonche. 41Vilombo navo vida wachoka ambili wawo ndikuyalila kwa mkuwo ndi kunena, "Iwe ndi mwana wa Mulungu!" Yesu adawakalipila vilombo ndi wadapaloleze kukamba, chifuko adajiwa kuti lye wadali ndi Kristo.42Nyengo kudatokucha, wadepita malolopande wandhu. Magulu ya wandhu yadali kumfunafuna ndi adaja pamelo adalipo. Adayesa kumchekeleza asadapita kwakutali ndi anyilwo. 43Nampho adakambila, "Kuti ndilalike nkhani za bwino za ufumu wa Mulungu pa mijhi yena yambili, pakuti iyi ndenda ade nidatumidwa pano." 44Ndipo wadaendekela kulalika mkati mwa sinagogi pa Uyahudi ponche.

Chapter 5

1Idachoke yapo wanthu adamkusikila ndi kumzungulila Yesu ndi kuvechela mau la Mulungu, pamene wadaima mbali mwa nyanja ya Genesareti. 2Wadayaona mabwato yayakulu yawili yaima mmphpete mwa nyanja. Ovua adachoka mmabwatomo ndikuchuka makoka yao. 3Yesu wadalowa mbwato umoji udali wa Simoni ndi kumpempha waupeleke bwato mmaji patali pang'onondi kuchidya ndipo wadakala ndi kuyaluza kuchokela m'bwato.4kukamba wadamkambila Simoni, "Upeleke bwato wako kujiwe ndikuchicha makoka yako uvue nchomba." 5Simon wa dayamkha ndi kukamba, Ambuye tachita nchito usiku onche, ndi sitidagwile chilichonche, nampho kwa maulanu, sinichiche makoka. 6Yapo adachita chimwecho adakusa nchomba zambili ndi makoka yao yadayamba kudukana. 7Kwa icho adaatana achianjao nibwato wina uja aje kuatangatila, adaja adajaza mabwato yonche, mbaka zimayamba kubila.8Nampho Simoni Petro, yapo wadaona chimwecho, wadagwa mmaombono mwa Yesu ndikukamba chokani kwanga, ndande ine ndi munthu ochimwa Ambuye." 9Ndande wadadabwichidwa, ndi onche adali pamoji ndiiye, kwa kavuidwe ka nchomba adachita. 10Ichi chidachitika pamoji ndi Yakobo ndi Yohana wana Zebedayo, adali ogwilizana ndi Simoni. Yesu wadamkambila Simoni, "Osaopa, ndande kuyambila chapano ndi kuendekela siuvue wanthu." 11Yapo adakweza mabwato yao kuchidya adasiya kila kanthu ndi kumchata iye.12Idachokela yapo adali mmuji wina wake, munthu wadaja makate wadali kumene, yapo wadamuona Yesu, wadagwa ndi kukotamicha nkhope mbaka panchi ndi kumpempha, kukamba, "Ambuye ngati mufuna mukoza kunichilicha." 13Yesu wadatambasula janja lake ndi kumkavya, ndi kukamba, "Nifuna. Chilika." Nthawi imweyo makate yadamsiya.14"Wadamkambila usadamkambila munthu walionche, nampho wadamkambila, "Mapita ukajilangize kwa anchembe ndi uchoche nchembe ya kuchila kwako ngati chija wada chilamula Musa.15nampho nkhani zimkuza iye zinaenela kwa kutali kupunda, ndi gulu la wanthu lidaja pamoji kumvechela ndiwayaluza ndi kuchilicha watenda yao." 16Nampho nyengo ndinyengo wamajipatula kuchengezi kupempha.17Idachokela siku limoji mu siku zimene wamatoyaluza, ndi adalipo Afarisayo ndi oyaluza matauuko adakala pamenepo adachokela ukondi uko mchigao cha Galilaya ndi Yudea, ndi kuchokela ku muji wa Yerusalemu. Mphavu yu Ambuye idali pamoji ndi iye kuchilicha.18Wanthu akumoji adaja, ambala pa mphasa munthu opoloza, ndi adafuna njila yo mlonja mkati kuti amgoneke panchi pachogolo pa Yesu. 19Siadapate njila yomlovya mkati ndande ya gulu la wanthu, kwa icho adakwela kuchindu ndi kumchicha yuja munthu panchi, kupitila mphasa yake pakati kati pa wanthu, pachogolo pa Yesu.20Ndi wapenya chikulupi chao Yesu wadakamba, "Bwenji, machimo yako wakululukidwa.'' 21Olemba ndi Afarisayo adayamba kufuncha limenelo ndi akamba, uyu yani wakamba matukwano? Yani wakoza kukululukila machimo ingakale Mulungu yoka?"22Nampho Yesu ndi wajiwa chiya ni icho aganizila, wadaayankha ndikuakambila ndande chiyani mfunchane ichi mkati mwa miti mayanu? 23Chiti chosalimbe kukamba, machimo yako yakululukidwa, kapena kukamba, 'Ima uende?' 24Hampho mjiwe kuti Mwana wa Adamu wali malamulo pajikola panchi yokululucha machimo, nikukambila iwe, uka, utenge mphasa yako ndi upite kukomo kwako."25Nthawi imweyo wadauka pamaso pao ndikutenga mphasa yake ija wadagonela. Ndi kupita kukomo kwake ndi waakuzika Ambuye Mulungu. 26Kila mmoji wadadabwichidwa ndi adamkuzika Mlungu. Adajala mantha, ndi kukamba taona vinthu ivo sitidavizewelele lelo."27Vatochokela vimenevo, Yesu wadachoka kumeneko, wadamuona osonkhecha watanidwa Lawi wakala pamalo po sonkhechela sonkho, wadamkambila, "Nichate." 28Kwa icho Lawi wadaima ndi kumchata, ndi kusiya kila chinthu kumbuyo.29Ndipo Lawi wadokonja pwando lalikulu ndanda ya Yesu. Adali osonkecha ambili kuja ndi wanthu ambili adakala pamoji ndikudya nao. 30Nampho Afarisayo ndi olemba wao amaadandaulila opunzila, ndi kukamba, ndande chiyani mkudya ndi kumwa ndi osonkhecha ndi wanthu wina ali ndi machimo?" 31Yesu wadaayankha, "Wanthu yao saadwala saafuna mchiliso ndi anyiwaja adwala oka nde samfune mmoji. 32Sinidaje kuatana wanthu amalinga kuti apemhe akululukidwile nampho yao ali ndi machimo.33Adamkambila, "Opunzila a Yohana kambili amamanga ndi kupempha ndi opunzila a Afarisayo nao achita chimwecho. Nampho opunzila wako akudya ndi kumwa." 34Yesu wadaakambila, "Ikozeka munthu walionche kuachita yao apita kuukwati akale osadye nyengo ali pamoji ndi mwene? 35Nampho masiku siyafike nyengo mwene ukwati yapo siwakale osadya."36Ndipo Yesu wadakamba mwa chifanizo. "Palibe uyo wa ng'amba nchalu ya chapato kuikila chigamba nchalu ya kale, wakachita chimwecho. Kudula nchaluya chapano siilana ndi ija nchalu ya kale.37ndi palibe munthu watenga divai ya chapano ndi kutila mmbiya za kale ngati wakatila ija divai ya chapano siiswe mbiya zonche ndi divai yene siimwazike ndi mbiya siziwanangike. 38Nampho divai ya chapano tauko itilidwe m'mbiya za chapano. 39Ndi palije uyo wakumwa divai ya kale ndi kukumbila divai ya chapano, ndande wakamba ija ya kale nde ya bwino."

Chapter 6

1Chipano idachokela ku Sabato kuti Yesu wadapita pakati pa munda wa vakudya ndi opuzila wake adali n'kucha vipacho, adivipu kusa pukusa pakati pa manja yao adadya vakudya. 2Nampho wena wa Afarisayo adakamba, kwa chiyani muchita chinthu icho chili osati cha tauko la zene kuchichita siku la Sabato"?3Yesu wadaayankha, wadakamba simudasome po chijha Daudi wadachita yapo wadali ndi njala, iye ndi waachimuna anyiyao adali pamojhi nae? 4Wadapita pakati pa nyumba ya Mulungu, ndi wadaitenga mikate yoela ndi kuidya baadhi, ndi kuichocha injake kwa wanthu anyiyao wadali nao adadya, ata ngati idali halali kwa anchembe kuidya." 5Potela wadaakambila, "Mwana wa Adamu ni Ambuye Asabato."6Idachokela Pasabato injake kuti wadapita mkati mwa sinagogi ndi kuwayaluza wanthu kumeneko. Padali ndi wanthu mmojhi jhanja lake la kwene lidali lopoloza. 7Olemba ndi Afarisayo amampenya bwino kuona ngati wadakamlamicha munthu siku la sabato, dala akoze kupata ndande ya kumshitaki kwa kuchita kulakwa. 8Nampho wamajhiwa chiyani amachiganizila ndi wadakamba kwa munthu uyo wadali opoloza jhanja, "Uka, ima yapa pakati kati pa kila mmojhi." Chimwecho yujha munthu wadauka ndi kuima pajha.9Yesu wadakamba kwa anyaiwo, "Nikufunchani anyaimwe, chazene siku la Sabato kuchita ubwino kapena kuchita kuipa, kulamicha umoyo kapena kuuwananga? Pothela wadaapenya onche ndi kumkambila yujha munthu, 10"Nyosha jhanja lako, wadachita n'chimwecho ndi jhanja lake lidalama. 11Nampho adajhalidwa ndi mpwai adakambichana okhaokha kukhuza chiyani afunika achite kwa Yesu.12Idachokela siku zimenezo kuti wadapita kuphili kupempha. Wadaendekela usiku onche kumpempha Mulungu. 13Yapo udali umawa, wadaatana opuzila wake, ndi waadaasankula kumi ndi awili pakati pao, anyiyao adatanidwa, "Atumiki."14Majhina yao anyiwajha atumiki yadali Simoni (uyo wadamtana Petro) ndi Andrea m'bale wake, Yakobo, Yohana, Filipo, Bartolomayo, 15Mathayo, Tomaso na Yakobo mwana wa Alfayo, Simoni, uyo wadatanidwa Zelote, 16Yuda mwana wa Yakobo ndi Yuda Iskariote, iye wadamng'anamukila.17Ndipo Yesu wadachika nao kuchokela kuphilindi kuima pamalo pa kwawa. Idadi ya ikulu ya opuzila wake adali kumeneko, pamojhi ndi idadi ya ikulu ya wanthu kuchokela ku Uyahudi ndiku Yerusalemu, ndi kupwani ya Tiro ndi Sidoni. 18Adajha kumvechela ndi kulamichidwa matenda yao. Wanthu anyiyao amachauchidwa ndi vihyuka voipa adamichidwa nao. 19Kila mmojhi pa msonkhano umeneo wadaesa kumgwila kwa ndande ya mphavu zake zidali zimachokela mkati mwake, ndi wadaalamicha onche.20Potela wadaapenya opuzila wake, ndi kukamba mwapachidua mwawi anyaimwe muli amphawi, kwa chifuko ufumu wa kumwamba ni wanu. 21Mwapachidwa mwawi anyaimwe muli ndi njala saazino chifuko simukutichidwe. Mwapachidwa mwawi anyaimwe mulila saazino, kwa chifuko simusekelele.22Mwapachidwa mwawi anyaimwe wanthu sakuipileni ndi kukupatulani anyaimwe kuti ni oipa, kwa chifuko cha mwana wa Adamu. 23Yangalilani pakati pa siku limenelo ndi kudumpha dumpha kwa chisangalalo, kwa ndande simukale ndi sawabu yaikulu kumwamba, kwa ndande achaatate wao wadaachitila n'chimwecho olosa.24Nampho ole anyaimwe muli opata! Kwa chifuko mwathopata chisangalalo chanu sazino. 25Ole wanu mwakhuta saazino, kwa chifuko simuone njala pambuyo, ole wanu museka saazino! Kwa chifuko simudandaule ndi kulila pambuyo26Ole wanu, yapo simuyelekedwe ndi wanthu onche! Kwa chifuko atate wao wadaachitila olosa aunami n'chimwecho.27Nampho nikamba kwanu anyaimwe munivechela, akondeni adani wanu ndi kwa achila ubwino anyiyao akuipilani. 28Apacheni mwawi anyiyao akulangani anyaimwe, ndi apempeleni anyiwajha akundani.29Kwa uyo wakubula chakaya limojhi, mng'anamulile ndi lakawili, ngati munthu wakakulanda jhoho usadamkaniza ndi kanzu. 30Mpache kila uyo wakupemha Ngati munthu wakakulanda chinthu icha chili chako usadampempha wakubwezele.31Ngati mukonda wanthu akuchitileni, namwe achitileni n'chimwecho. 32Ngati mukonda wanthu akukondeni anyaimwepe chimwecho nde thawabu yanji kwanu? Kwa ndande ata amachimo waakonda anyiwajha waakonda anyaio. 33Ngati simwachitile ubwino anyiwajha akuchitilani anyaimwe ubwino, chimwecho nde thawabu yanji kwanu? Kwa chifuko ata amachimo achita n'chimwecho. 34Ngati simukongoleche vinthu kwa wanthu, anyiyao muganizila saakubwezeleni, chimwecho nde thawabu yanji kwanu? Ata amachimo waakongolecha amachimo.35Nampho akondeni oipa wanu ndi achitileni ubwino. Ndi akongolecheni ndi msadaopa kukhuza kubwezedwela thawabu siikale aikulu. Simukale wana wa uyo wali kumwamba kwa chifuko iye mwene ni wabwino kwa wanthu opande kuyamikia ndi olakwa. 36Khalani ndi lisungu, ngati atate wanu umo ali ndi lisungu.37Msadalamula, namwe msadalamulidwa. Msada aleswa namwe msaleswedwa. Alekele ni namwe simulekeleledwe.38Apacheni wina namwe simupachidwe kiasi cha ulemu icho chachindilidwa, kusukidwa sukidwa ndi kutaika - taika pa maombono panu. Kwa chifuok cha chipimo chali chonche icho mutumikila kupimila, chipimo chimwecho sichitumike kuupimilani anyaimwe.''39Pothela wadaakambila chifanizi nampho. "Bwanji bwanji munthu uyo wali osapenye wakhoza kumuona munthu mwina osapenye? Ngati wachita n'chimwecho basi onche adakatila njhenje, bwanji sadakabila? 40Upuzila siwakala wamkulu kumpitilila puzisi wake, nampho kila munthu wakata yaluzidwa kwa chazene siwakale ngati puzisi wake.41Ndi kwachiyani basi akapenya chipatwa chili mkati mwadiso la m'bale wako, ndi boliti ilo lili mkati mwa diso lako siuliona? 42Siukoze kumkambila m'bale wako, 'M'bale nipempha nichichoche chipatwa chili mkati mwa diso lako,' nawe siupenya boliti lili mkati mwa diso lako umwene? Mnafiki iwe! Poyamba lichoche boliti ilo lili mdiso mwako wa mwene ndeyapo siuone bwino kuchocha chipatwa chili mdiso la m'bale wako.43Kwa ndande palibe mtengo wa bwino ubala vipacho voipa, palibe mtengo oipa ubala vipachp vabwino. 44Kwa chifuko kila mtengo ujiwikana kwa vipacho vake. Kwa chifuko wanthu siakucha tini kuchokela mminga, wala sa akucha mizabibu kuchokela mmichongoma.Munthu wa bwino pakati pa kusunga kwa bwino kwa mtima wake yachoka yayo yali ya bwino ndi munthu oipa pakati pa kuikila yoipa ya mtima wake yachoka yayo yali yoipa kwa chifuko mkamwa mwake wakamba yajha yajhala mumtima mwake.46Kwa chiyani munitana, 'Ambuye, Ambuye', Ndi mukali simuyachita yajha niyakamba? 47Kila munthu uyo wakujha kwanga ndi kunivechela mau yanga ndi kuyachitila nchito, sinikulangizeni umo wali. 48Walingana ndi munthu uyo wamanga nyumba yake, iye wakumba panchi kupunda, ndikumanga msingi wa nyumba pa mwala wa chiimile. Kusapukila yapokudajha chigumula cha majhi yadaibula nyumba nampho siidakoze kutingizika kwa chifuko idamangidwa bwino.49Nampo waliyonche walivela maula ndi kulivecha, chifanizi chake ngati munthu wadamanga nyumba yake pamwamba pa dothi yapo padalibe msingi, mchinje yapo udachika kwa mphavu, nyumba ijha idatopata kugwa papakulu.

Chapter 7

1Badala ya Yesu kumaliza kila chintu ichoamafuna amakamba kuti wantu yao amamvechela, adalowa ku Kapernaumu.2Kapolo fulani wakida oyawadi ndithamanida na kwaiye, wadali wodwala kupunda ndi wadali pafupi ya kufa. 3Nampho ikadala wavela kuhusu Yesu, Akida wadamtuma mfumu wakiyahudi, kumpemba waje kumtangatila kapolo wake ili siwadafa. 4Yapo achafika pafupi ndi Yesu, adamngwila kwa mphavu ndi kukamba, wasitahili kuti ifunika kuti kuchita chimwechi kwa ajili yake, 5kwa fukwa wadakonda jiko lantu, ndi uzidamanga kanisa kwa ajili yantu."6Yesu wadaendekela ndi ulendo wake pamoji nao. Nampha kabla siwadapite papatali ndi nyumba, afisa mmoji wadatuma mabwenji wake kukamba nayo. "AAmbuye simdajilemecha mawene kwa chifuko ine. 7Kwa chifukwa ichi sinikuganizila hata ine namwe ne kunti nifai kuja kwako, nampho kamba mau utndi wanchinto wanga siwalame. 8Kodi ine nane muntu ndaikidwa kwachinto nina wankondo panchi panga. Kukama yuncha hueita ndi kupita kwa mwina "Uje naye uje kwa mtumishi wanga huchita haki naye kuchita.9Yesu yapowadavela yano wadazizwa ndi kuwa ng'anamukila, makutano anyio wamachota ndikukama." Nikukumbilani, hata pamoji ni Israeli, sindidawahi kupenya muntu walindi imani yaikulungati uyu. 10Ilawaja anyiyao adatumidwa kubwela kukomondi kumpeza mtumiki wadili wa moyo.11Fulani pambuyo payaya, wadachokela kodi Yesu wadali kusafiri kupita mnji udatanidwa Naini. Wanafunzi wake wadapitanao pamoji naye wadayambana ndi umati wa wantu. 12Yapowadafika pafupi ndi komolajiji kapenya, muntu uyowafa wali obalidwa, ndimwana wapayoka kwa mama wake. Uyowadali mjane ndi umati wachifitikuchoka kwachijiji adali pomaji nae. 13Yapoadamuona, Ambuye wadamsendelela ndilisungu lalikulu kwa basi pamwamba pake ndi kumkambila, "usidalila". 14Kisha wadasendela pachogolo wadaligafya bokosi lilo adatengela ntupi, ndi waja adatenga adaima ndikukamba "Mnyamata ndikamba uka" 15Ohuka wadanyanyuka ndikukala panchi ndikuyamba kukumba. Kisha Yesu akamkabidhi kwa mama yake.16Nampho manta yada jala onche adaendelea kumuyamika Mulungu adakamba "Nabii wa mkulu wakwezedwa mtima mwatu" ndi Mulungu waapenya wantu wake" 17Izi ngani zawino za Yesu zinaenela Yudea yonchendi kwa jiko lapafupi.18Opuzisa wa Yohana wadakambila vintu ivivonche. 19Ndi Yohana wadatana awili wo opuzisa wakendikwa atuma kwa Ambuye kukamba "Iwendeyuja wadaja, aukuli muntu mwina timlindilile? 20Yapo adafikapafupi ndi Yesu anyiyawa adakamba, "Yohana mbatizaji watituma kwakoti kambe, 'Iwendi yuja wadaja aukuli muntu mwina timpenyelele?"21Ndi nyengo imeneyo wadalamicha wantu ambili kuchoka matendo ndi masauko, kuchoka kwa roho za ukazuzu, ndikw awantu ndi vipofu wadapachakupenya. 22Yesu wadayanka ndikukamba kwao. "Pambuyo pakuti mdapita ukomdachoka simjuwiche Yohana ichomwachiona ndikuchivela. Alivipofu salandile kupenya ndiviwete aenda, amakatesatakosike, micheka avela akufa safufuliwa ndikukala amoyotena, makapuku sakambidye maiyabwino. 23Ndi muntu walienche siwasie kuniamini ine kwa chifukwacha vichito vanga."24Baada ya anyiwaja adatumidwa ndi Yohana kubwela uko adachoka, Yesu wadayamba kukamba kwamakutano pamwamba pa Yohana, "Mdapita kubwalo kupenya chiyani, mwazi ukakala utingizikandi mphepo? 25Chipano mdapita kubwlao kupenya chiyani, muntu uyowavalabwino? Penyani wantu waja anyiwaja avala vivalo vachifalme ndikulama maisha ya chisangalalo alipokunafasi za kifalme. 26Nampho mpita kubwalo kupenya chyani, Nabii? Etu, ndikukamba kwanu ndi zaidi sana kuliko nabii.27Huyu nde wadalembedwela nkani yanga pachogolo pamaso yenu, uyosiwokonje njila kwande yanga, 28Nikamba kwanu, kati yaanyiwaja anyiyao adabadwa ndi wamkazi, palibe wamkulu ngati Yohana nampho muntu siwakala wa muhimu sana uyosiwalamendi Mulungu pamalo walipo iyee, siwakale wamkulu kuchepa Yohana."29Ndi wantu onche yapoadavela ya yapamojindi wachocha ushuru, adatangazakuti Mulungu nde mwene malumulo. Adalipokati yao waja adabatizidwa kwa ubatizowa Yohana. 30Nampho mafarisayo ndi ataalamu wa sheria za Kiyahudi, ambao sadabatizwe ndi iye adakana hekima za Mulungu kwajili yao achinawene.31Chipano ndikoza kuwafaniza ndi chiyani wantu wakazazi ichi? Alibwanji hasai? 32Alingana ndiwana yaosowela kueneo lasoko, anyiyao angokala ndi kutanana mmoji baada yamwina naokamba, tapuliza filimbi kwachiko chanu, ndisimdavine ndikuombele ndisimdalile.'33Yohana mbatizaji wadaja ndisiwadadye mkate walakumwa mvinyo, ndi mdakamba "Wali ndi pepo. 34Ndi mdakamba "Pamoji wajawadya ndikumwa jela mbwenji. 35Nampho ulemu ujilangiza kuti ulindi haki kwa chiwana wake onche."36Mmoji wa Mafarisayo wadampempha Yesu wapite kudya pamoji ndiiye. 37Penyani kudali ndi wamkazi mmoji katika jiko limenelo uyowadali ndi dhambi. Adamgundua kuti wadali wakali kwa farisayo, wadapeleka mchupa yamanukato. 38Wadaima kumbuyo kwake pafupi ndi myendo yake uku ndi walila. Tena wadayamba kukatapicha myendo yake kwa misozi, ndi kuichangula kwa machichi yamutu wake, wadaibusu myendo ya ndikuipaka manukato.39Ndiyuja farisayo uyowadali wadamlalika Yesu yapowadapenya chimwecho, wadaganiza mwenewake wadakamba, ngati uyumuntu wadakakala nabii, wadakajiwa uyu ndi yani ndi waina yanji ya wamkazi uyo wamgafya, pakuti mwene dhambi. 40Yesu wadankandi kumkambila, "Simoni ndili nichintu cha kukukambila. "Wadakamba" "Chikambe tu mpuzisi!"41Yesu wadakamba "Wadalipo ndi odaidwa awili ndi wokongolecha mmoji. Mmoji wadali wa madadwa dinari miano ndiwakawili wamadaidwa dinari hamsini. 42Ndiyapo adali alibe ndalama yakumlipa adale kelela onche. Chipano ndiyani siwakwade kupunda? 43Simoni wadyanka ndikukamba, "Nigeniza uyo waleke leledwa kupunda." Yesu wadamkambila, "Walamula kwa uhalali."44Yesu wadamng'anamkila wamkazi ndikukamba kwa Simoni, "Umpenya uyu mkazi. Nalowa mnyumba yako. Siudanipache maji kwachifuko cha mnyendo mwanga, Nampho uyo, kwa misozi ya wadakatapicha myendo yanga ndi changula kwa machichi yake. 45Siudanibusu nampho iye kuchoka yapowadolowa muno siwadisie kunibusu myendo yanga.46Siudaipake myendo yanga mafuta, nampho udaipaka myendo yanga kwa manokato. 47Kwa chintu achi, ndikukambila kuti wadalipondi dhambi kwa mbili ndi walekeleledwa.48Pambuyo wadamkambila wamkazi, "Dhambi zako zalekeleledwa" 49Waja akala pameza pamoji naye adayamba kukambaa achinawene kwa chinawene, "Huyu ndiyani hadi waalekelela dhambi?" 50Ndi Yesu wadamkambila wamkzi, "Imani yako ya kutandiza mapita kwa mtendele"

Chapter 8

1Idachokela nthawi yaifupi pambuyo kuti mpulumusi wadayamba kuenda katika miji ni vijiji vosiana siana, kulalikila ni kutangaza nkhani ya bwino ya ufulu wa Mulungu ni waja kumi ni awili adapita pamoji ni iyi, 2naoncho wachikazi akuti adali alamichidwa kuchoka kwa mzimu yoipa ni matenda yosiana siana. Adali Mariamu watanidwa Magdalena. Uyo wadali wachochedwa mizimu saba. 3Yohana mkazake wa kuza ni meneja wa Herode, Susana, ni wachikazi wina ambili achocha chuma chao chifuko chao achina wene.4Ni baada ya umati wa wanthu kujikusanya pamoji akakalapo ni wanthu adaja kwa iye kuchoka miji yosiana siana, wadakambana nao kwa kutumia malangizo. 5"Ovyala wadapita kuvyala mbeu,yapo wamavyala, baazi ya mbeu zimenezo zidagwela pamphepete pa njila zidapondedwa panchi pa myendo, ni mbalamiza kumwamba adazija. 6Mbeu zina zidagwa pamwamba padoti la myamba ni yapo zidapondedwa panchi pa myendo, ni mbalamiza kumwamba adazija.7Mbeu zia zidagwela padali mitengo ya minga, nayo mitengo ya minga idakula pamoji ni zija mbeu zidavinikilidwa. 8Nampho mbeu zina zidagwela padali doti la bwino ni zidabala vakuja mara mia zaidi. "Baada ya mpulumusi kukamba mambo yaya, wadakamba kwa sauti, "Waliyonche wali ni masikio yovela ni wavele."9Nao opuzila wake adamfuncha mate ya langizo limenelo, 10Yesu mpulumusi wadakambila, "Mwapachidwa mwawi oijiwa chisisi cha ufumu wa Mulungu, nampho wathu wina siayaluzidwe tu kwa langizo, dala kuti akapenya asidaona ni akavela siadaelewa.'11Ni iindo mate yalanizo ili. Mbeu ni mau la Mulungu. 12Mbeu zija zidagwa mphete mwa njila ni anyiwaja wanthu alivela mau, ni pambuyo oipa satana walitenga patali kuchoka minitima, dala kuti osakulupalila ni kulamichidwa. 13Nampho ni zija zidagwela papili ni wanthu waja avela mau ni kulilandila kwa chisangalalo nampho aliji mizizi yaliyonche, akulupalilape kwa muda wa ufupi, ni wakati wa maeso akugwa.14Ni mbeu zija zidagwela paminga ni wanthu avela mau, nampho yapo aendekela kukula avimikilidwa ni nchito ni chuma ni ubwino wa maisha yaya ni siabala matunda. 15Nampho zija mbeu zidagwela padoti la bwino ni waja wanthu, anyiyao ochika ni mitima ya bwino, baada yovela mau aligwilila ni likala bwino ni kubala matunda ya kuembekeza.16Chapana, palije ata mmoji, wawasha taa ni kuikuchika kwa bakuli au kwika panchi pa chitanda. Badala ya kuiika pamwamba pa taa dala kuti kila mmoji uyo walowa wapate kuiona. 17Pakuti palije chakujibisa icho sichijiwikana, au chalichonche chili chobisika icho sichijiwika chikakala kuli dangalila. 18Kwa icho kala openyelela yapo ukala uvechela. Kwa ndande wali nacho, kwa iye siwaongezeledwe cha mbili, nampho uyo walije ata chija chaching'ono wali nacho chitengedwe."19Pambuyo mama wake Mpulumusi nachabale wake adaja kwa iye siadawandikile chifuko cha unyinji wa wanthu. 20Niwadakambidwila, "Mama wako ni achabale wako ali yapo pabwalo afuna kukomana ni iwe. 21Nampho, Mpulumusi wadayamkha wadakamba, "Mama wanga ni achabale wangu ni anyiyao alivela mau la Mlungu ni kulilemekeza."22Idachokela siku limoji, kati ya siku zija Mpulumusi ni opuzila wake adakwela mbwato, ni wadakambila, "Yifombokelechija la kawili lanyanja." Andaa matanga yao. 23Nampho yapo adayamba kuchoka, Mpulumusi wadagona litulo, ni mwela wamkulu ni mphepo, ni boti lao lidayamba kujala maji ni adali katika hatari yaikulu sana.24Pambuyo oluzila wake adaja kwa iye nikumuucha, adakamba, "Abwana mkubwa! Tili pafupi kufa!" Wadauka nikuukanipila mphepo ni mafunde ya maji vidasia ni kudakala kwatulia. 25Niwadakambila, "Chikulupi chanu chili kuti?" Adaopa, adazizwa, adakambichana kila mmoji ni njake, "Uyu ni yani kiasi kuti walamula ata mphepo, ni maji vimlemekeza?"26Adafika muji wa Gerasini uli upande wa kumbuyo wa Galilaya. 27Mpulumusi yapo wadachika ni kuponda pa nthaka, munthu mmoji kuchoka kumjini, wadapezane nae, ni uyu munthu wadali ni mphavu za kumdima, kwa muda wautali wamavale nchalu, ni wadali siwamakale mnyumba, nampho wamakala kumakaburi.28Yapo wadamuona Mpulumusi, wadalila kwa sauti, ni wadagwa panchi pachogolo pake, kwa sauti ya ikulu wadakomba, nachita chiomi kwa iwe, Mpulumusi mwana wa Mlungu wali kumwamba? Nikupempha usanibula ine" 29Mpulumusi wadalamula mzimu oipa umchoke munthu yuja, chakuko mara za mbili yamtesa. Ata ngati wadali wamangidwa mnyororo ni kubanidwa ni kuikidwa panchi pa oimilila, wadadula vifundo ni kuendechedwa ni mzimu mpaka kupili.30Mpulumusi wadamfuncha, "Jina lako yani?" wadayankhe wadakamba, "Legioni" Chifuko mizimu ya mbili yalowa kwa iye. 31Adaendekela kumpempho usati lamula tipite kulijenje.32Gulu la nguruwe lidali liwesedwa kumwamba kwa pili, adampempha, waruhusu akalowe kwa zija nguruwe. Ni wadaruhusu kuchita chimwecho. 33Kwa icho ija mizimu idamchoka munthu yuja ni kulowa kwa zija nguruwe, ni lija kundi lida tamanga mpaka pamwinuko wa pili mpaka kimyanja ni zida bila mmenemo.34Anyiwaja wanthu adali kuwesa zija nguruwe yapo adaone chachitika, adatamanga ni adachocha taarifa paja pamjini ni kubwalo katika miji yazungulila. 35Wanthu yapo adavela yamaneyoadapita kupenya icho chachokela, ni adaja kwa Mpulumusi ni ada muona munthu uyo mizimu wadali yamchoka. Wadali wavala bwino ni wali jnalu za bwino, wakala pa myendo ya pulumusi ni adaopa.36Nde yapo mmoji wao yapo wadaone chachitika wadayamba kwa fotokozela wina umo uyu munthu wadali wachogozedwa ni mizimu umo walamichidwila. 37Wanthu onehe amkoa wa Wagerasi no malo yazungulila adampemphe Mpulumusi wachoke kwa anyiio kwa ndande adali ni kuopa kwa mbili, ni wadalowa mbwato dala kubwela.38Muthu yuja zidamchoka mzimu wadampempha Mpulumusi kupita nae, nampho Mpulumusi wada mkambila wapite ni kukamba, 39"Bwela kunyumba yako ni uwelenge yaja yonche yayo Mlungu wakuchitila" Uyu munthu wadachoka, niwatangaza ponche katika muji onche yaja yonche yayo Mpulumusi wayachita kwa chifu kwa chake.40Ni mpulumusi wadabwela, wanthu adamkaribisha, kwa ndande onche amato mlindilila. 41Ponya wadaja munthu mmoji watanidwa yaino ni mmoji kati ya ochogoza katika nyumba ya mapemphelo. Yairo wadagwa mtendo mwa Mpulumusi ni kumpempha wapite kukomo lake, 42chifuko wali ni mwana wa mkazi mmoja tu, wadali ni msinkhu wa vyaka kumi ni viwili, ni wadali katika hali osati ya bwino. Ni yapo wamapita, wanthu adali aunjikoma zidi yake.43Wamkazi uyo wamachoka mwazi kwa vyaka kumini viwili wadali pamwepo ni wadatumia ndalama za mbili kwa waganga, nampho palije uyo wadamlammicha ata mmoji, 44wadaja kumbuyo kwa mpulumusi ni kugusa mkunjo wa kanzu lake, ni gafula kuchoka mwazi kudasia.45Mpulumusi wadakamba, "Yani uyo wanigusa?" Yapo adakana onche, Petro wadakamba, Bwana Mkubwa, umati wa wanthu akusukuma ni kukuzungulila." 46Nampho Mpulumusi wadakamba, "Munthu mmoji wadanigusa, chafuko nidajiwa mphavu zachoka mtupilanga."47Wamkazi yapo wadaona kuti siwakoza kubisa icho wachita, wadayamba kutenthemela, wadagwa panchi pachogolo pa Mpulumusi ni kutangaza pamaso pa wanthu onche ndande izo zamchita wamguse ni umo walamila gafla. 48Baadae wadanena kwake, "Mwali, chikulupi chaku chakuchita ukale wa moyo. Mapita kwa mtendele."49Yapo wamaendekela kukamba, munthu mmoji kuchoka kunyumba ya ochogoza nyumba ya mapemphelo, wadakamba, "Mwali wako wafa. Usamsaucha mwalimu." 50Nampho Mpulumusi yapo wadavela chimwecho, wadamu yankha, "Usaopa. Kulupalila tu, ni siwalamichidwe."51Nampho yapo wadalowa mmenenao mnyumba, siwadamruhusu munthu waliyoehhe kulowa ni iye, ikapanda Petro, Yohana ni Yakobo, Baba wake mwali ni mama wake. 52Chapano wanthu onehe adali kudandaule ni kuchocha sauti chifukwa cha iye, nampho wadakamba, "Msabula pokoso, wadafe, nampho wando gona tu." 53Nampho adamseka kwa zarau, niajiwa kuti wafa.54Nampho iye, niwamgwila mwalijanja, wadatana kwa sauti, wadakamba, "Mwana, inuka" 55mzimu wake udambwelela, ni wadainuka muda umweo. Wadalamulila kuti, wapachidwe chinthu chakuti dala kutiwaje. 56Obala wake adadabwa, nampho wadalamula siadamkambila munthu icho chidachokela.

Chapter 9

1Wadaatana anyiwaja kumi ndi awili pamaji, wadani nkha kukezandi malamulo pamwamba pa mizim yonche ndi kulamicha kudwala. 2Wadaatuma apite kutangaza ulemelela wa Mulungu ndi kulamicha adwala.3Wadakambila, "Msidatenga chalichanche ndande ya ulande wanu wala chiboka, wala mkoba, wala mkate, wala hela wala msidatenga nchalu ziwili. 4Nyumba yaliyanche iyosimkalawe, mkhale mmene mo mpaka yapo simcheko pamalo pamonepo.5Ndi kwaanyiwaja sakulandilani, yapo simchake pa muji umeneo, jikung'untheni lifumbi mmyenda yanu kwa kulangizila pamwamba pao." 6Adachaka ni kupita kupitila vijiji, ndi kutangazamau ya bwino ni kulamicha wanthu kila pamalo.7Chipana Herode, olemekezedwa, wadavela yonche yayo yamachakela wadaganizila sana, ndande idakambikandi baazi kuti Yohana abatiza wahyuka pakati pa akufa, 8ndi baazi Elia watachakela ndi kwa wina kuti mmoji wa aresa akale ahyuka pakati pa akufancha. 9Herode wadakamba, "Nidamchinja Yohana, nampho uyundi yani ni vela nkhani zake? Ndi Herode wadafunafuna njila ya kumwona Yesu.10Nyengo adabwela anyiwaja adatumidwa, adamkambila kila chinthu icho achichita. Wadaatenga pamoji ndiye, wadapita yonka pakati pa muji utanidwa Bethsadia. 11Nampho wanthu ada vela kupitila limonela adamcheta, ndi wadakalibisha, ndi wadakamba na kuhusu ulemelelo wa Mulungu, ndi wadalamicha anyiwaja adafuna kulamichidwa.12Siku imayamba kuntha, ndi anyiwaja kumindi awili adapita kwake ndi kukamba, "Atawanye wanthu kuti apite mvijiji va jirani ndi mmijini akafunetune popumulilandi chakuja, ndande tulipamalo pa ntengo." 13Nampha wadakaambila, "Anyiimwe anikheni chinthu cha kuja." Adakamba "Tilibe zaidi ya vipande visana va mikate ndi nchomba ziwili, nampa tudakapita ndi kugula chakuja ndande ya mkusanyika uu wawanthu." 14Kudali ndi wachimuna ada lika elfu zisano paja. Wadakambila opuzila wako. "Ankhalicheni panchi kupitila vikundi va wanthu afikila hamsini kwa kila chikundi.15Ndi adachita mchimwechandi wanthu adankhalapanchi. 16Wadatenga mikate isano ndi nchamba liwili ndi wadaponya kamwamba, wada vibariki, ndi kuvimeza kupitila vipande, wadaaninka apuzila wako ili aviike pachagalo pa wanthu. 17Wonche adakhuta, ndi vipande va chakudya ivo va khalila vidatoledwa ndi kujazidwa mvikapu kumi ndi viwili.18Ndi yapo idali kuti, yapo wamapempha yanka pe, opulila wake adali pamanchi naye, ndi wadafuncha wadakamba, "Wanthu akamba ine ndi yani?" 19Adajibu, adakamba, "Yohana obatiza, nampha wina akamba Eliya, ndi wina akamba mmenchi wa olosa anyengo za hale ahhuka ncha."20Wada akambila, "Nampha anyiimwe mkamba ine ndi yani?" Wadajibu Petro wadakamba, "Kristo kuchoka kwa Mulungu." 21Nampho kwa kuwakaniza, Yesu wadaelekeza siadamkambila waliyenche pamwamba pa limenelo, 22Wadakamba kuti mwana wa munthu lazima wateseke kwa vinthu vimbili ndi kukanidwa ndimidala ndi wakulu anchembe ndi olemba, ndi siwapedwe, ndi siku yakatatu siwahyuke.23Wadakambila wonche, "Ngati munthu waliyanche wakafuna kunichata lazima wajikane mwene, wakatenge mtanda wake kila siku, ndi wanichate. 24Waliyenche oyowaesa kuyalamicha maisha yake siwayataize, nampho waliyenche wataiza maisha yake kwa faida yanga, siwayaokoe. 25Bwa sichimnthandize chizani munthu, ngati siwapate jikha lanche, nampho wataiza au wapata asala ya mtima wake?26Waliyanche uyasiwanianele nchani ine ndi mau yanga, kwake iye mwana wa munthu siwamuonele nchani yapo siwankhala katika ulemelelo wake, ndi ulemelelo wa atate ndi angela oyela. 27Nampha nikukambilani uzene, kuli baadhi yanu aima yapa, saonja kufa mpaka aane ulemelelo wa Mulungu."28Wadachakela pakati pa siku nane baada ya Yesu kukamba mau yameneyo kuti wadatenga pamoji nae Petro, Yohana na Yakobo, adakueda kupili kupempha. 29Ndi yapowadali kupitila kupempha, kuonekana kwa nkhope yake idabadilika, ndi nchalu zake zidali zaela ndi kupulikila.30Ndi penya, kudali wachimuna awili amankamba naye! Wadali Musa ndi Elia, 31adaone kana kupitila ulemelelo. Adakamba kuhusu kuchaka kwake, chinthu ambacha wadakhalibia kuchimaliza ku Yerusalemu.32Chipano Petro ndi anyiwaja adali pamoji naye adali pakati pa litulo lizita. Nampha yapoadauka, adauena ulemelela wake ndi wachimuza awili anyiyawo adaima pamoji nae. 33Idachokela kuti, yapoamachoka kwa Yesu, Petro wadamkambila, "Mbuye, ndi chabwina kwatu kunkhala yapa ndi ifunikana tukonche pakala wanthu atatu. Tukonche limoji kwaajili yako, limoji kwa ajili ya Musa, ndi limoji kwaajili ya Eliya." Siwadaelewe ichaamaengelea.34Yapo wamakamba yameneya, udaja mtambo ndi kwa vinikila, ndi adaopa yapoadaona azungukidwandi mtamba. 35Sauti idachaka mmitamba idakamba, "Uyu ni mwana wanga achagulidwa. Mvencheleni iye." 36Sauti yapaidakhala kachete, Yesu wadali yokha pe adakhala kachete, ndi kupitila siku zimeneza siadamkambile waliyonche lalilonche mkati mwa yaja ayaona.37Siku iyo idanchotela, baada ya chaka kupili gulu lalikulu la wanthu lidapezananaye. 38Penya, wamuna kuchaka ku mkusanyiko wadalila kwa sauti, wadakamba, "Oteluza nikupempha umpeye mwanawanga, pakuti nde mwana wanga yakha pe. 39Uona mtima oipa ugwila, ndi nyengo imweyo kubula pakasa, ndi kumchita wachanganyikiwe ndi kuchakedwa ndipovu kukamwa. Naka kumchaka kwa shida, ndi imchiticha hupwetekedwa sana. 40Ndida pempha apulila wako kuikalipila ichake nampho siadakhaze."41Yesu wadajibu wakamba, "Anyiimwe chibadwa chasa khurupalile ndi icho cha wanangika, mpaka zikulanchi sindi khale namwe ndi kutengolana namwe? Jina ya mwana wako pana." 42Mnyamata wamata kuncha, mtima aipa udamgwecha panchi ndi kumtingila kwa funcho. Nampho Yesu wadaukalipila uncha mtima oipa, wadamlamincha mnyamata, ndi kumninka kwa atate wake.43Onche adashangaa ndi ukulu wa Mulungu. Nampho amate shangaa wanche kwa vinthu vonche ivo vidachitika, wadakamba kwa opuzila wake, 44"Mau yakukhaleni mmakutu mwanu, pakuti mwana wa munthu siwachonchedwe mmancha mwa wanthu." 45Nampho siadaelewe mate ya mau yameneyo, ndi yadabisidwa pamasa pao, ili siadancha kuelewa. Adaopa kumfuncha kuhusu mau zameneyo.46Ndeyapo kukambinchana kudayamba pakati pao kupitila yani siwakhale wa mkulu. 47Nampho Yesu yapo wajiwa icha amakambi lana mmitimo mwao, wadamtenga mwana wa mng'ana ndi kumuika bendela lake, 48ndi wadakamba, "Ngati munthu waliyonche wakamlandila mwana wa mng'ona ngati uyu kwa jina langa, wanilandila ine ncho, ndi waliyonche wakanilandila ine, wamlandila ncho uyawanituma, pakuti uyo wali wamng'ene pakuti panu wenche nde uye wali wa mkulu"49Yohana wadajibu wadakamba, "Ambuye, tudamue na munthu ni wachocha mzimu kwa jina laka ndi tudamzuia, ndande siwali ndi ife." 50Nampho Yesu wadakambila, "Msidamzuia, pakuti uyesiwakupingania mmeneyo ndiwanu"51Idachokela kuti, kulingana na ndi siku umazimanka libia siku lake la kupita kumwamba, kwa uimala wadapenya masa yake Yerusalemu. 52Wadatuma wanthu pachagora pake, naoncha adapita ni kulowa kupitila kijiji cha Wasamaria ili amuadalie malo. 53Nampho wanthu kumeneka siadamlandile, ndande wadapenya masa yake ku Yerusalemu.54Opuzila wake Yakobo ni Yohana yapo adaliona limenelo, adakamba, "Ambuye mfuna tulamule mato uchike panchi kuchoka kumwamba uwapyeleze?" 55Nampho wadang'anamukila ndi kwa tutumila. 56Ndipo adapita kijiji china.57Yapo amapita kupitila njila yao, munthu mmoji wadamkambila, "Sinikuchate palipanche upita." 58Yesu wadamkambila, "Galuwamntonga walini maenje, mbalamila za mwamba zili ni visa, nampha mwana wa mwanadamu walibe paganeka mutu wake."59Ndo wadamkambila munthu mwina, "Nichate." Nampho iye wadakamba, "Ambuye, ni loleze huti nipite nikamzike tate wanga," 60Nampha iye wadamkambila, "Asiye akufa amzike wa kufa wao, nampha iwe mapita ukatangaze ufumu wa Mulungu kila pamalo."61Nampha cha munthu mwina wadakamba. "Sinikuchate, Mbuye, nampho ni loleze huti ni kalaile anyiyawo ali mnyumba yanga." 62Nampha Yesu wadamkambila palibe munthu, wantila janja lake kulima ndi kupenya mmbuyo uyasiwafai kwa ufumu wa Mulungu."

Chapter 10

1Pambuyo pake, Ambuye adasankha anjake sabini, ndikwatumiza awili awili kuti achogolele kumujhi walionche ndi malo alioneke iye wadafuna kupita. 2Waadaakambila vinthu vambili, nampho ogwila nchito ndi ochepha. Kwaicho muphempheni Mbuye wa nchito, kuti wapeleke msanga anchito.3Pitani mmijhi. Onani, ndikhutumani ngati mbelele pakatikati pa agalu amthengo. 4Msatenga tumba la ndalama, kapena chikwama cha paulendo, kapena sapato, ndi msalonjelana ndi waliyenche mmnjila.5Nyumba yaliyonche iyo simulowemo, payamba kambani, mtendere ukhalemo mnyumba muno.' 6Ngati walimo munthu wa mtendere, mtendere siukha kwa iye, nampho ngati osati mtendere siukhubweleleni. 7Nampho mnyumba imeneyo, idyani ndi kumwa icho sachichoche, mate yake kuti wanchito waenela malipilo yake. Msachoka nyumba iyi kupita nyumba ina.8Mujhi walionche ilo simulowe ndi kulandilidwa, idyani chalichonche icho sichichokhe pachogolo panu, 9ndi lamichani odwala onche alimnyumba imeneyo, kambani kwa anyaio ufumu wa Mlungu wakufikilani pafupi'10Nampho mujhi walionche uwo simulowemo, ngati simulandilidwa, tulukani pitani pa njila ndi mkambe, 11'Ingakhale lifumbi lilimmapazi mwatu tilikung'untha nampho jhiwani kuti, ufumu wa Mlungu wawandikila.' 12Ndakukambilani kuti siku lachilango silikhale la chiweluzo Mlungu siwachiteko chifundo polanga Sodoma kuposa mujhi ujha.13Ole wakho iwe Korazini, ole wakho Bethsaida! Ngati nchito za chitika mkati mwako zikada chitika ku Tiro ndi Sidoni, akadaomboka khalelemwe. 14Nampho mulungo siwachite chifundo pa sikhu lolanga Tiro ndi Sidoni kuposa pakukulangani. 15Iwe Kapernaumu, Uganiza kuti siukwezedwa mbakana kumwamba? Iyayi, siuchichidwe panchi mbakana kwa akhufa16Uyosiwa kuvele anyaimwe wandivela ine, ndi waliyenche uyo siwakhukane ni wandikana ine, waliyenche uyo siwandikane ine wamkana uyo wandituma"17Anyiwajha sabini adabwela ndi chimwemwe ndikukamba, "Ambuye, ingakhale mizimu yoipha yativela mwa jhina lanu." 18Yesu wadaakambila, "Ndidamuona Satani wadagwa kuchokela kumwamba mwamba ngati mphambe. 19Onani ndakupachani mphamvu zopondela njoka ndi chipilili, ndi mphamvu zonche za adani, ndipalijhe chalichonche kwa njila yaliyonche icho sichikhupwetekeni. 20Msakhondwe pa izi, kuti mizimu yoipha yakivelani, kondwani kupunda pakuti maina yanu yaembedwa kumwamba."21Ntawi ijha wadakondwa kupunda mwa mzima Oyera, ndikunena, ndikuelekela iwe, atate, Ambuye akumwamba ndi jhiko, chifukwa wabisa izi kwa wanthu anjelu ndi omphuzira, kundi vunukula izi kwa wanthu osaphumzira ngati wana waang'ono ang'ono. Yao, atate pakuti adakondwera pamaso pao."22"Atate adaika vinthu vonche mmanja mwanga, ndi palijhe uyo wajhiwa mwana nde yani ila atate, ndi palijhe uyo wajhiwa atate ndi ayani ila mwana ndi waliyenche wali mwana wakhumbila kujhivunukula kwa iye."23Wanang'anamukila omphuzira wake, ndi kukhamba nao chisili, "Adalisidwa yawo aona izi muziona anyaimwe. 24Ndakukhambilani anyaimwe kuti olosi ambili ndi mafumu adakumbila kuona izi muziona, ndisadaone, ndikuvela yayomuyavela, ndisadayavele."25Onani mphuzisi wakuti wa malamulo ya yahudi wadaima ndikunuyesa ndi kunena, "Mphuzisi ndichite bwaji kuti ndilowe mumoyo wa muyaya?" 26Yesu wadamkambila, mmalamulo chalembedwa chiyani? Uwelenga bwanji?" 27Wadayankha, ndikunena ukonde chauta Mulungu wako wonche, ndi mpha mvu zako zonche, ndi njelu zako zonjhe, ndi wapafupi wako mkonde ngati umo ujhikondela umwene." 28Yesu wadakamba wayankha bwino, chita chimwecho ndi si ulame."29Nampho mphuzisi, wadakhumbila kujiwe lengela kuti iye olungama, wadamkhambila Yesu, "Kuti wapafupi wangayonde yani?" 30Yesu wadayankha ndi kunena, "Munthu mwina wamachokela ku Yerusalemu ndi kupita ku Yeriko. Wadagwela kwa wanthu achifuamba, adamlanda chuma chake ndikummenya ndikumusia pafupi kumwalila.31Mwa mwawi wanchembe mwina wamachika njila imweijha yapho wadamuona wadalambalala. 32Chimozimozi mlawi mwina yapho wadafika pajha ndi kumuona naye wadalambalala.33Nampho wakusamaria mmojhi, yapowadali paulendo wadapita pajha wadali munthu yujha. Yapowamwona wadamlengera lisungu. 34Wadamsendelela ndikummanga vilonda vake, wadamwazira mafuta ndi vinyo, adamukweza pamwamba pabulu wake ndikupita naye, kunyumba ya lendo ndi kumsamalila. 35Siku lidachatila wadatenga dinari ziwili wadampacha mwene nyumba ndikumkambila, Msamalila chalichonche chopitilila sindijhe kulipila yaposindibwele.'36ndi yuti mwaatatu yawa, uganiza, wadali waphafupi wake iye wadagwela mkati kati mwa achifwamba?" 37Mphuzisi wadakamba, yujha wadalangiza lisungu kwa iye." Yesu wadamkambila, mapita ukachite chimwecho."38Yapo adali pa ulendo, adalowa mujhi wina, ndi wamkhazi mmojhi jhina lake Martha wadamandila kukhomo lake. 39Wadali ndi mkhulu wake wamatani dwa Mariamu, uyo wadakhala pa miendo ya Ambuye ndikuvechela mau lao.40Nampho Martha wamachita nchito zambili zokonjha chakudya, wadapita kwa Yesu, ndi kukamba, "Ambuye, simusamala kuti mkuluwanga wandisiilandekha nchito? Kwaicho mkambileni wanditangatile." 41Nampho Ambuye adamuyankha, ndikumkambila, "Martha, Martha, uchauchika pakati pa zambili, 42nampho chinthu chimojhipe chamate. Mariamu wasankha chili chabwino, icho sichichochedwa kwa iye."

Chapter 11

1Yapoidafika ndawi Yesu yapo wamape pamalo pina, mmoji wa opuzila wake wadakambila, "Ambuye, tiyaluze ife kupembela ngati Yohana umo wamayaluzila opuzila wake'.Yesu wadauza, yapompembela, kambani, 'Atate, jina lanu lielesedwe. Ufalme wanu bwele.3Mutunikhe sikono watu wakila nyengo. 4Mtukululukile muchimo yatu, ngati ife umo tukululukila onje atilakwila. Msidatichogoza pa maeso."5Yesu wadauza, "Ndi yani kwanu siwakale ndimbwenji, uyo siwampitile usiku, ndi kukambila, mbwenji nibweleke masikono yatatu. 6Pandande mbwenjilanga wanifikila saazino kuchoka paulendo, ndi ine ndilibe chakwakonjela.' 7Ndi yuja wali mnyumba wadamuyakha, usidanininga mavuto, chicheko chato chekedwa, ndi mwana wanga, pamoji ndi ine tutogona pachitanda. Chindikoza kuuka ndi kukunikha iwe masikono. 8Ndikuuzani, ngakale siwauka ndi kuminikha ine masikono ngati bwe njilake, pundande yoendekela kupwanyila bila njoni, siwauke ndi kukupacha viduke vumbili va musikono kulingana ndi chifuno chako.9Nane nikukambilani, pembani namwe simuningidwe, funani, numwesipachidwe, bulani odi namwe simasulidwe. 10Pakuti kila mundu uyo wapemba siwalandile, ndi kila muntu uyo wafuna siwapate, ndikila mundu wabula odi, chicheko si chimasulidwe kwaiye.11Ndi tate yuti mmalo mwanu, mwanawake wakapemba njombo ndikunikha foka baada yake? 12Pina kupemba zila ndikupacha chi pilili baada yake?. 13Pandande, ingakale imwe mulioipa mujiwa kuti wana wanu mboto zabwino, bwaji simboto za atute watu akuniwa kuti sakuningeni mtima oyela yao apemba?"14Pambuyo, Yesu wadali wamapembela vimbuza, ndi vimbuza wadali ngo mundu wali ndivimbuza ndi mundu wadali ndi vimbuza wadali ngo nda ndipo vimbuza yapo vidamchoka, mundu mmeneyo wadakoza kukamba, ambili amamdabwa kupunda. 15Nambo wandu wina amakambilana, uyu wachocha vimbuza kapa Beelzebul, wakulu wa vimbuza16Wina amamuyesa ndikufuna walangize chinunu kuchoka kumwamba. 17Nambo Yesu wadayajiwa makhanizo yao ndi kwakambila, "Kila mfumu uwo sakhawike sukalendikukala ndinyumba iyo yakhawika siigwe.18Ngati Satana siwakale wakhawika, ufulu wake siuimebwaji? Pandande mkamba nichocha viwanda pa Belzebuli. 19Ngati ine ni chocha viwanda kwa Belzebuli bwa anjunu achocha viwanda pajina lanji? Pandande iyi, anyi iwo sakulamueni anyiimwe. 20Nambo, ngati ni chocha viwanda ndi chalu cha Mulungu, basi ufulu wa Mbuye watifikila.21Munthu wambavu wali ndizida yupo walonda nyumba yake, vindu vake, si vikale bwino. 22Nambo yapo siwavamilidwe ndi mundu uyo walini mbavu zambili yuja mundu walindimbavu siwamulande zida zake, ndi kuzitenga vyuma vake vonje. 23Iye wakana kukala ndi ine wali kumbuye nane, ndiiye uyo siwadasake pamoji ndiine wavimwaza.24Chiwanda chichafu yapochimchoka mundu, chipita ndikufunafuna pamalo palibe ndi maji ili chipumulile. Yapo siwakale walakosa, chikamba, 'sinibwele uko nachoka. 25Yapo sichibwele ndikupeza nyumba yalambulidwa ndiyakala bwino. 26Ndipo chipita ndi kufuna viwanda saba vili voipa kuposa iye mwene ndi kwapeleka aje akale pamalo paja pa wandu mmeneyo wakala oipa kuposa mmayambo mwake."27Idachokela kuti yapo wamakamba mau yameneyo, opuila mwina wadakuza mau yake pamwamba pa onje pa msongano wawandu ndi kukamba lilemekezeke mimba ilo lakubala ndi mawle wayumwa" 28Nambo iye wadakamba, abalikidwa anyiwao avela mau ya Mulungu ndikulisunga.29Nambo unyinji wawandu amabwela ndi kuchuluka, Yesu wadayamba kukamba "Chibadwaichi ndichibadwa choopya. Ukufuna chinunu, ndinalibe chinunu iyo saningidwe kupunda ndija chinunu cha Yona. 30Ndipo ngati Yona wadali chinunu kwa wandu Aninawi, chocho ndimwana wa Adamu umosiwakalile chilangizo kwa mbadwa uu31Malikiya wakusini siwaime siku la malamulo ndi wandu mbadwa wachopano ndikwalamula anyiiwo, ndipo iye wadachoka potela pajiko ndipo waje wavechele ulemu za Solomoni, pano walipo wali wakulu kuposa Solomoni.Wandu aku Ninawi saime pabamulo pamoji ndiwandu ambadwa chino sikula malamulo salamule, ndio anyiiwo adalapa kwa mapembelo yayona, ndi penya, yapa walipo wakulu kuposa Yona.33Palibe mundu walioje, wawasha nyali ndikuiika pamalo papanji pali ndi mdima uwosiuoneka au panji pamseche, nambu wawasha ndikuika pamwamba pachindu ili kila mundu walowa wapeze kupenya kuyela. 34Maso yako ndinyali latupi diso lako likakala labwino basi tupilako lonje silikale poyela. Nambo diso lako likakala loipa basi tupilako silikale pamdima. 35Sopano, kalani chonga ndi kuyela muli mkati mwanu usidatilidwa mdima. 36Ndipo basi, ngati tupi lako lonje uli umwene kuyela, ndi palibe pamalo ili pakati pakuyela, ndipo tupilako silikale ngati nyali iwala ndi kuchocha kuyela kwanu."37Yapowadamaliza kukamba, Farisayo wadakambila wakaje chakuja mnyumba mwake, naye Yesu wadalowa mnyumba ndi ndi kukala pamoji ndi iwo. 38Ndi Mafarisayo adadabwa pakuti ivosi wasambe huti pambuyo pa chakuja chaujulo.39Nambo ambuye wadakambila, "Anyiimwe Mafarisayo mchuka kubwalo kwa vikombe ndi mbale, nambo mkuti mwanu mwajala janje ndi vinduvoipa. 40Anyiimwe wandu mulibe ndi njelu, bwaiye wadalenga kubwalo siwadakoje ndi mkati njo? 41Aninngeni olumala yali mnyumba, ndivindu vonje sivikale bwino kwanu.42Nambo ole wanu Mafarisayo, pakuti mchocha sembe ya mnana ndi mchicha ndikila aina za ndiyo ya mmunda. Nambo mwasiya vindu vauzene ndi kumkonda Mulungu. Ndi bwino kupunda kuchita yali yaubwino ndi kumsangalasa Mulungu, bila kusiya kuchita ndi vina vo.43Ole wanu Mafarisayo, pakuti mukonda kukala pamipando yapachogolo mnyumba ya Mulungu ndikulonjeledwa kwa moni za ulemu musika. 44Ole wanu, ndipo mulingana ndi viliza vilibe chilangizo ambavu wandu aenda pamwamba pake popande kujiwa."45Mpuzisi mmoji wa malamulo ya Kiyahudi wadamuyakha ndikukambila, "Mpuzisi, icho uchikamba chitiipicha ife." 46Yesu wadakamba, "Ole wanu, apuzisi amalamulo! Ndipo mwanikha wandu katundu yayosakoza kunyamula, nambo anyiimwe simuigusa makatundu yo ata mmoji wa vyala vanu.47Ole wanu, pa ndande mmanga ndikuik achizindikilo mvizila va alosi ovo adapendwa ndi midala yanu. 48Ndipo ndanyiimwe mpenya ndi kuvomelezana ndi njito adazichita midala yanu pa ndande imeneyojo, ulemu wa Mulungu ikamba, sindikutu mileni mlosi ndi mbusa nao sakuteseni ndukukupani wena wanu.49Kwa sababu hiyo pia, hekima ya Mungu inasema, 'Nitawatumia manabii na mitume nao watawatesa na kuwaua baadhi yao. 50Chibadwa hichi sihiyangile pamwazi walosi yaoapedwa tangu kuyamba kwa jiko, 51kuchoka pamwazi wa Abeli hadi mwazi wa Zakaria, uyo wadapendwa pakati pa madhabahu ndi pachilungamo. Ndipo ndikuuzani anyiimwe, chibadwa ichi sichiyangile.52Ole wanu apuzisi a malamulo za Ayahudi, pandande matenga ki za ulamulilo; machinawene simulowa, ndiyao afuna kulowa mwakaniza."53Pambuyo pa Yesu kuchoka paja, atumiki ndi Mafarisayo adamkana ndi kukanilana naye pakati pavindu vambili. 54Amaesa kunkamba pamau yake.

Chapter 12

1Paufawi imeneyo waufu ambili adakanila limoji mpaka ada fikira kupondena wadayamba kukanga ndi oyaiuzidwa wakepoyamsa, "Jisingeneni ni mau yoipa ya Mafrisayo yamene yali yo ng'ana mkang'anamka"2Ndipadelijepo choufu cho jibisa chimene sichidema sulidwe wala akani idebiswidwa yosaoneka. 3Chilichonche mwachi nena kundima silivechedwe paliwala ndi yaliyonche mwayakamba mmakutu uka simwa nyumba vyau vya mkati vamangidwa sivikambilidwe pamwamba pa chufula nyumba.4Ndikukangilani ma bwanjilanga msada waopa akupa fupi udipotela aaje chintu chene chochota, 5Nampho siudi kukanizeni lumeneyo wafunika kuwopa mwopeni yuja pambuyo pakuti wapa walindila milo la kukupelekani malo yoopa nde nikukambilani anyi umwe muopei mmeneyo.6Bwanji mbamwezi sano siziguli chidwa kwa ndelama ziwili? Inga kale chimwecho palije ata mmoji wau siwayawalilidwe pa chogolu la Mulungu. 7Nampho mujiwe kuti machichi ya mifu yanu yawalengedwa msada opa anyiimwe muliamate kupunda mbala ne zaambia.8Ndikukambilani mmenyo siwandivemale ive pamaso pa wantu, Mwana wa Adamu siwa muende pachogoro pa malaika wa Mulungu. 9Nampho waliyenche siwandikana pamatapa wantu watenche siwakanidwe pachogoro pa angelo a Mulungu. 10Waliyenche siwakambe mau yoipa pamwamba pa mwaka wa muntu siwalekeleledwe nampho waliyeude siwakembe voipa kwa mzimu woyele siwa lekeleledwa.11Yapo siiakupelekani pa chogoro pawa akurakuna kanisa achogoleli ndi ndi olamulila msada opa mtundu wokamba pakujikambilila kapena chiyani si mchikambe, 12Chifuko mzimu woyela siwafiyaluze mtaade umeneo simkambile paufawi imeneyo."13Muntu maoji paguru wade mkambila mwalimu mkambile mbalewanga wandigawile malo yo siidwila kwanga." 14Yesu wademuyauka yani wandi ika kuti ndikale olamula ndi oilanicho pakasikatipanu? 15Nde pamene wade atambila, "Jipenyeleleni ndi mtundu walionche ofuine vosufunidwa chifu kwa kulama kwa muntu sikuli pa kati pavintu vimene walinavo."16Yesu wada akambila chifanizi wadakamba munde wamutu mmoji opata lidabala kwambili kupunda, 17ndiwadefuncho mkati mwake ndiwakaamba ndichife chiyani chifukwa ndilike malo yaika vakudya vanga? 18Sindi chife chimwe sindi wanange. Nkokwe zanga za zing'ono ndikumanga nkkwe yaikuru ndi kuikavakudya vanga vonhe ndi vintu vene vonche. 19Sindiukambile moyo wanga, moyo wajiikira vintu vambili vyaka vyambili pumulila, udye, umwe, nde kusangalala."20Nampho Mulungu wade mkambila iwe muntu siujiwachochita usikuwalelo au funa mtima wako kuchokela kwako ndi vintu vonche wavikonje sivikale vachiyani? 21Nde umo sikalile kwa muntu wali yenche wajiikila vopata ndisiwa jikonja chifukwa cha Mulungu.22Yesu wada akambila uchafira wake mmwemo ndi kukambilani msada kala ndimauta pakati pakula makwanie kuti sindye chiyani kapewa pamwamba pa mafupi yanu kuti si mvale chiyani 23Chifukwa kulama ndi kupunda chakudya ndifupi ndikuponda kwa kuvala.24Mpenye mbalame za mlengalenga sizilima. Kapena kukorola zilife nyumba kapena nkokwe zoikila nampo Tata wanu kudyechani anyi imwe si abwino kupunda mbalame! 25Yani mmeneyo pakatikati panu mwene siwaji chanche siwakoza kujiongezela mkwamba umoji pakati pa kulama kwake? 26Ikekakala ngati simkoza kuchita chimwecho chintu cha ching'ono chili chokozeka chifuko chiyani kuyavu tikila yaliyena?27Yapenyeni maduwa mme yakuti kumela siyachita nchito kapena kuji nyembeza, nampho ndikukambilani ingakale Sulemani pakasi kati pa ufuru wake wonche siwada valichidwe ngati yamoji yapo ya yaya, 28Ngasi Mulungu wayavalicha bwino mechamba ya mmakunde yamene lelopalije ndimana yafaidwa pamoto bwanji osufi kupunda akuvalichani anyaimwe anyaimwe muli ndi chikurupililo chaching'ono!29Msada chachika pamwamba pakuti simudye chiyani kapena simumwe chiyani wala simdakola ni mauta. 30Pakuti meiko yonche yapanchi achau chika ndiyameneyo ndi Atata wanu ajiwa kuti muyafuna ya meneyo.31Nampo ufunefu neni ufuro wa Mulungu poyamba ndiyameneyo yena simchulu chilidwe, 32msade opa anyiimwe muliguru lochepa chifuko atatawanu asangalala kukupachani nyaimwe ufuru umeneo.33Gulicheni vintu vanu vonche ndi mkaapache osauka ujichifile matumba yosata__kujiokila kumwamba yosata pamalo pamene aukungu sakoza ku sendelela kapene vichulo sivikoza kuwa nangika. 34Pakuti pali kujiikizila kwako ndiye pamene palimtima wako si ukalepo.35Chalu zanu zazitali zikale za mangidwa kwa malamba ndi nyali zanu zipenyaleledwe kuti zili zowala, 36ndi mkale ngati wantu ampenyelela mkuru wao kuchokela ku chikondwa lelo cha ukwati dalakuti wakafika ndi kubula hodi sakoze kummafulila chicheko mwamsanga.37Awanengikidwa anyowapa ogwira chito achamene mkuru wao wawapeze alimaso chazana siwa mange ncharu yake yaitali kwa lamsa pambayo siwakaliche panchi kwache kudya ndipambuyo kwa fandiza. 38Ngati waulam siwaje kwa kawili kwa ulinda wa usiku kapene kakatatu kawada ndikwapeza ajikonja siikale bwino kwa achemene ogwira chinto.39Yoende kida payameneyo mjiwe mwene nyumba wakodojiwa utawi mnkungu wakuja siwakadakuzo kulamula nyumba yake imangidwe. 40Mkale chonga pakuti simujiwa ntawi yangu mwana wa Muungu siwabwete.41Petro wadanena, "Wamkuru uti kambila ta achina wefe vifanizi ivi kapena umkambila kila muntu? 42Wamtaru wadakamba yani wali utunidwa okuropalidwa kapena odekamfima mmene wa mkuru wake siwamuike pamwamba pa ogwiro chifo wena dala kuti wa agawile chakudya chao ntawoyofunika? 43Wali ndi mwawi ugwila nchitu yuja mwe wamkuru wake wakafika siwampeze ndi wachita nchito imene wada kambilidwa. 44Chezane ndikukambilani si mugaike pamwamba pa chuma chake chonche.45Nampo ogwira nchiso yoja wakalamba pa mtima pake wamkuru wanga wa chedwa kufika mmwemo wakayamba kwa abula ogwila chito wa achimuna ndi wa achikazi pambuyo kuyamba kudya ndikumwa ndi kulojela, 46wamkuru wake yuja wanchito siwaje ntawi yosajiwika neyemche siwadulidwe vipinjiri vipinjiri ndiku ikidwa malo yapamoji ndi osa kurupilika'47Ogwira nchito wajiwa chikondi cha wamkuru wkaa na yenche siwadekonje ndikuchita bwino bwia ndichikondi chake siwabulidwe vikosi vambili. 48Nampho ogwira nchito mwe siwajiwa chikonchi cha wamkuu wake napo wakochitu chime chifunika pakuchita pake siwa bolidwe vikutu vochepa chifueko iye wade pachidwa vambili vambili vifunika kuchokela kwaiye ndiye wada kurupilila vambili sivifunike vambili kupuada vambili sivifunike vambili kupuanda.49Naja kuukweleza moto pajiko nikombila ukale wato kwelela, 50Nampo ndili ndichilangizo cholangizidwa ndichoodande ulicha mpaka pamene siuziadikalidwe!51Bwanji mganiza kuti naja kupeleka mtende lepajiko? Iyai ndikukambilani pambuyo paka ndapeleka kusandukililana. 52Kuyambila chapani ndikuyendekela sikukale ndiwantu asano pakasi pa nyumba imoji asandukililana ndi atatu siakale osakalilana ndiawili ndi awili siakale osakalilana ndi atatu. 53Siasaudukalilana atate siakala asaudula likana ndimwanawake ndimwana siwakele wasandukilalana ndi tete wake mama siakale asandukilana na mwana wake wamkazi ndi wana wa mkazi siwakale wasandukelanene ndi mamawake Apongozi siasandukililane ndi mpongoli wao.54Yesu wama ukambila msonkano, "Yapo simuone mitambo ichakala kuzambwe kwajiko mkamba ntawi za vule za wandikila ndi mmweno ikalila. 55Ndi mpepo ya kumwela ikayamba mkamba sikukale kutenda kwambili ndimo ikalila. 56Anyiimwe osakurupalika mkoza kutambulila kulangulika kwa jiko ndi kuwala nampo ikula bwaaji si mkoza kutumbulila ntawi ilipo?57Ndande yanji tumoji mmoji wanu siwakoza kujiwa lililabwino kwaiye kulichita utani walindi ntawi yochita chimwecho? 58Chifuko mkapita ndiwa mlandu wako pachogolo pa olamule milandu figwilozile kugwilizana naye mkali mkuanda mnjira osukola wakupeleke kwa olamula mlandu ndi ola mula mlandu wakakakupeleka agwililila lamula akokuika kundende. 59Ndekukambila siuchoka kumemeko mpakaulipe ndalama zotele.

Chapter 13

1Panyengo imeneyo, padali ndi akumojhi wandhu adampachanghani pamwamba pa Agalilaya yawo Pilato adawapa ndi kusingizana mwazi wao ndi nchembe zawo. 2Yesu wadayankha ndi kumkambila, "Bwanji muganiza kuti Wagalilaya ameneo adali ndi machimo kupitilila Wagalilaya wena wonche nde chifuko akomanidwa ndi viopa vimenevo? 3Iyayi, ni kukambilani, nampo, ngatiosalape, na mwencho simlete chimwecho.4Kapena wandhu kumi na nane pa Siloamu yawo mtolondi udagwa ndi kuwapa, mganiza anyilwo adali ndi machimo kupunda kupitila wandhu wena mu Yerusalemu? 5Iyayi, ine ninena, kuti ngati mkalapa, amjiimwe mwa wonche namwe simute.6Yesu adakambila chifanizi ichi, "Mundhu mmojhi wadali ndi mtengo udavyalidwa pa munda wake nde wadapita kufunafuna vipacho mmwamba mwake nampho siwadavipate. 7Wadamkambila osunga bustani, 'Pemya, pa vyaka vitatu najha ndi kuyesa kufuna vipacho mu mtini mmenemo nampho sinapate. Uudule. Ndande chiyani uwanange ndhaka?8Osunga bustani wadayankha ndi kunena, 'uusiye chaka chino ndipo niulimilile ndi kuika mbolea pamwamba pake. 9Ngati siupache vipacho chaka chikujha, ni bwino; nampho nati siupacha uudule!"10Chipano Yesu wadeli mkuyaluza pa imojhi yamasinagogi pa nyengo ya Sabato. 11Kapenya, wadalipo maye mmojhi uyo kwa vyake kumi na nane wadali ndi mzimu woyipa wa wonda, ndi iye wadali opiudika ndi opaude kujikozela nditu kuima.12Yesu yapowadamwona, wadamtana, kumkambila, "Amaye, mwaikidwa mmtendele kuchokela mkuonde kwanu." 13Wadaika manja yake kumwamba kwake, ndi pamwepo tuphi lake wadajiongola ndi kumpacha ulemelo Mulungu. 14Nampho wamkulu wa sinagogi wadakwiya kwa chifuko Yesu wadasi kumlamicha pa siku ya Sabato. Ndipo ohamula wadayankha kwakambila amsoghano, "Kuli masiku sita izo ndi cha mafinga kuchita nchito. Majhani kulamichidwa, osati msiku za sabato.'15Ambuye adamuyamcha ndi kunena, "Linami! Palijhe wa mmojhi wanyiimwe kumasula punda wake kapena ng'ombe kuchoka mkora ndi kwachogoza kwapeleka kumwa pasiku ya Sabato? 16Mmwemo msikana wa Abrahamu, uyo Satana wadammanga kwa vyaka kumi na nane, bwanji siwamafunike kunungidwa kwake kusadamasulidwa pa siku ya Sabato?"17Yapo wadali kunena mau yayo, anyiwaja wonche, adamkaniha adaona nchoni, namho amsoghano wonche wena adakondwa cha ndande ya vichito vo dabwicha adavichita.18Yesu adanena, "Ufumu wa Mulungu walingana ndi chiyani, ndi nikozakulinganichana ndi chiyani? 19Ndi ngati mbeu ya haradari iyo wadatenga mundhu mmojhi ndi kuivyala mmunda mwake, ndi kumela kukala mtengo waukulu, ndi mbalame za kumwamba adamanga visa vao pa nthawi yake.20Penancho wadanena, "Niufananize ndi chiyani ufumu wa Mulungu? 21Nde ngati yolujuka iyo wamkaze adaitenga ndi kusingizana mvopimila vitatu va ufa mpakana kutupama."22Yesu wadayendela kila mujhi nai chijiji mnjila kupita ku Yerusalemu ndi kuyaluza. 23Mundhu mmojhi wadafujha, ndi wandhu ochepa tu yawosiapulumuchidwe?" Nampho adakambila, 24"Limbicha kulowa kwapitila chicheko chowonda, chifuko ambili siayise siakoza kulowa.25Ndipo pambuyo uyimilila anyumba kuima ndi kumanga chicheko, ndipo simuime kubwalo ndi kumenya hodi pakomo ndi kunena, Ambuye, Ambuye, timasulileni iye siwayankhe ndi kwakambila, sindi kujhiwani anyiimwe kapena ukomchoka.' 26Ndipo simnene, Tidadya ndi kumwa pa maso pako ndi iwe udayaluza mmitaa yatu." 27Nampho iye siwayankhe, ndikukambilani, sinikujhiwani ukomchoka, chokani kwa ine, anyimw mchita voyipa!'28Sikukale ndi chililizi ndi kukukutamano nyengo yapo simwone Abrahamu, Isaka, Yakobo ndi olosa wonche pa ufumu wa Mulungu, nampho amjiimwe mwachinawene mwataidwa kubwalo. 29Siabwele kuchokela kuvuma, kuzambwe, kumpoto ndi kumwela, ndi kupuma pa meza ya chakudya cha ujhulo pa ufumu wa Mulungu. 30Ndi mjhiwe limenelo, wotela ndi oyamba ndi woyamba siwakale wotela."31Ntawi ya ifui pambuyo, wa amojhi wa Afarisayo adajha ndikumkambila, "Pita ndi uchoke pano chifuko Herode wafuna kukupa." 32Yesu adanena, "Mapitani mkamkambile yujha ghalutengo, pnya, natamangicha vilombo ndi kuchita kulamicha lelo ndi mawa, ndi siku ya katatu sinikwaniliche chopanga changa. 33Pa yaliyonche, ni malinga kwa chifuko changa kueudekela lelo, mawa ndi siku yokhatila, pakuti sivomeleka kumpha olosa kutali ndi Yerusalemu.34Yerusalemu, Yerusalemu, yaini akupa olosa ndi kwatimba myala ndi anyiyawo ahimidwa kwanu. Mara kangati nimafuna kukusanyani chiwana wanu ngati nkhuku umowakumbatila wana ankhuku panchi pa mapapiko yake, nampho simalifune limenelo. 35Kapenya nyumba yako yapelezedwa. Ndiine ni kukambila, simkoza kuniona ata yaposimnene 'Wapeza mawi uyo wakujha kwa jhia la Ambuye."

Chapter 14

1Idachokela siku la Sabato, yapo wamapita kukomo kwa mmoji wa mchogoleli wa Afarisayo kudya mkate, nao amamchatilila kwa pafupi. 2Pachogolo pake wadali munthu mmoji wama chauchidwa ndi chotupa. 3Yesu wadafuncha ojiwa mwa Wayahudi ndi Mafarisayo, "Bwa ndi malinga kumchilicha msiku la sabato, kapena lyayi?"4Nampho anyiiwo adali chete, kwa icho Yesu wadamgwila, wadamchilicha ndi kumkamba wajipita. 5Naye wada akambila, yani pakati panu wali ndi mwana kapena ng'ombe wakabila mchitime siku ya Sabato siwamchuula?" 6Anyiiwo saadakoze kuchocha yankho pa nkhani ija.7Nyengo Yesu yapowadajiwa kuti yao adatanidwa asankhula mipando ya ulemu, wadaakambila mwa chifanizo, ndi waakambila, 8"Yapo mtanidwa ndi munthu ku ukwati, usadakala mmalo mwa ulemu, ndande yake ikozeka watanidwa munthu olemekezeka kupunda. 9Wakaja mmene wakutanani wakoza kukukambila iwe mpatuke uyu pamalo pako, nde ukoza kuima kwa nchoni kupita kukala kumbuyo.10Nampho iwe ukatanidwa kakale pamalo potela, kuti yapo siwaje yuja wakutanani wakoze kukukambila iwe, bwenji pita kakale kuchogolo, ndeyapo siukale olewekezeka kwa yao wakala nao pameza. 11Chifuko uyo wajikweza siwachichidwe ndi uyo wajichicha siwakwezedwe.'12Yesu naye wadamkambila munthu uyo wadamtana, yapo uchocha chakudya chausana kapena chaujulo, usaatana mabwenji wako, kapenda abale wako, kapena amuji wanu, kapena apafupi wako achuma, kuti anyiiwo. Angakutane iwe ndi kupeza malipilo13Pambuyo pake yapo uchita pwando, atane osauka, olumala osaende, osapenye, 14ndi iwe siupeze mdaliso ndande saakoza kukupacha mkokolo, mateyake siupeze mkokolo mu chizyukililo cha wanthu amalinga."15Nyengo mmoji wa amjiwaja adakala pameza ndi Yesu yapo wadavela chimwecho nae wadamkambila wadalisidwa uyo siwadye mkate mu ufumu wa Mulungu!" 16Nampho Yesu wadamkambila, munthu mmoji wadakonja pwando ndi kutana wanthu ambili. 17Nyengo pwando latokonjeka, wadamtuma mtumiki wake kuakambila amjiwaja atanidwa, 'Majani, ndande vinthu vonche vatokonjeka.'18Onche adayamba kupempha mkulukilo, oyamba wadamkambila mtumiki, nagula munda, nifuna nikauone, chonde nikululukile.' 19Ndi mwina wadakamba, 'Nagula ng'ombe ndi ine nipita kuziesa, chonde ndikululukile.' 20Ndi munthu mwina wadakamba, nakwata wamkazi, kwa icho sinikoza kuja.'21Mtumiki wadabwela ndi kuakambila abwana wake nkhani imeneyo, yuja mwene nyumba wadakwiya ndi kumkambila mtumiki wake pita msanga mmiji ukaje nao pano osauka, osaende, osapenye, ndi olumala." 22Mtumiki wadakamba, abwana vonche mkambavo vatochitika mbaka chapano malo yakalipo.'23Bwana adamkambila mtumiki pita mmiseo ndi njila zazing'ono ukaachimize wanthu olowe mnyumba kuti nyumba ijale. 24Pakuti nikukambilani wanthu waja adatanidwa poyamba palije uyo siwalawe pwando langa.'25Chipano gulu lalikulu limapita pamoji ndi iye, wadang'ana muka ndi kuakambila, 26'Ngati munthu wakaja kwa ine siwambila tate wake, mai wake, mkazi wake, wana wake, abale wake wachinuna ndi wachikazi etu ndi moyo wake siwakoza kukala opunzila wanga. 27Munthu ngati siwatenga mtanda wake ndi kuja mmbuyo mwanga siwakoza kukala opunzila wanga.28Pakuti yani pakati panu wakumbila kumanga mnara siwakala kuwelenga ntengo icho chifunika chikwanile? 29Pina wakayamba kumanga ndi kulepela kusiliza, onche yao saaone saayambe kumseka, 30Nda akamba munthu uyu wayamba kumanga, ndi wadalije mphavu ya siliza.'31Kapena mfumu nji wakafuna kubulana ndi mfumu mwina mu nkhondo siwakala panchi ndi wanthu makumi elufu kubulana ndi mfumu mwina wali ndi wanthu makumi elufu ziwili? 32Ni ngati osati chimwecho nyengo asirikari awina akali kutali omatuma munthu kufuna mtendele. 33Kwa icho walienche pakati panu uyo siwasiya yonche walinavo, siwakoza kukala opunzila wanga.34Mchele wabwino, nampho ikakala wasukuluka ukozancho bwanji kukala wabwino? 35Ulijencho nchito kuyambila mdoti utaidwa kwa kutali, uyo walindi makulu wavele."

Chapter 15

1Basi okusanya usuru onche ndi wina anyiyao ali ndi dhambi adajha kwa Yesu ndi kumvechela. 2Ndi olemba ada dandaula ndi kukamba, "Munthu uyu wa akalibisha ali ndi dhambi ndi kudya nao."3Yesu wadakamba chifanizi ichi kwa anyaio, wadakamba 4"Yani kwanu wali ndi mbelele mia moja ndi wakasowedwa ndi imojhi wapo, siwazisia zijha tisiini ndi tisa mthengo, ndikuifuna funa ijha yasowa mbaka waione? 5Nae wakathokuipata siwaiike mmapewa mwake ndi kuyangala.6Yapo wadafika pakhomo, wadaatana mabwenji yake ndi majhilani wake wadakambila sangalalani pamojhi ndi ine pakuti naiona mbelele yanga iyo idasowa.' 7nikukambilani sinikhale ndi chisangalalo kumwamba kwa chifuko w dhambi mmojhi walapa, zaidi ya wene haki tisini ndi tisa anyiyao alibe ndande yo lapa.8Au kuli wamkazinji mwene sarafu kumi za ndalama, wakasowedwa sarafu imojhi siwakweleza nyali ndi kulambula nyumba ndi kufuna fuda kwa bidii mbaka yapo siwaipate? 9Ndi wakatoipata siwaatane mabwenji yake ndi apafupi wake siwaakambile sangalala ni pamojhi nane, pakuti naipatancho sarafu yanga idasoweza. 10Hata n'chimwecho nikukambilani kuli chisanga lalo pachogolo pa angelo a Mulungu kwa chifuko mwene zambi mmojhi walapa."11Ndi Yesu wadakamba, "Munthu mmojhi wadali ndi wana awili 12yujha wamng'ono wadaakambila atate wake, Atate nipacheni malo ya chuma changa iyoifunika kusiidwila. Chimwecho wadawananga chuma chake kati yao.13Siku osati za mbili yujha wamng'ono wadavikusanya vonche ivowamavimiliki wadapita jhiko la kutali, ndi kumeneko wadawananga ndalama zake, kugula vinthu ivo sivifunika, ndi kuwananga ndalama zake kwa chidekete. 14Nae yapo wadatotumikila vonche njala ya ikulu idalowa jhiko lijha nae wadayamba kukala pakati pofuna.15Wadapita kujhilembecha mwene kwa munthu mmojhi wa jhiko lijha, nae wadampeleka kumunda kwake kujechela nkhumba. 16Ndi wamakhumbila kujhikuticha kwa makowa yayo yamaja nkhumba, kwa chifuko palibe munthu wadampacha chinthu chali chonche wapate kudya.17Nampho yujha mwana wa mng'ono yapo wadaganizila mumtima mwake, wadakamba 'atumiki angati wa atate wanga ali ndi chakudya cha mbili cho kwana ndi ine nili pano, nikufa ndi njala! 18Sinichoke ndi kupita kwa atate wanga, ndi kwa akambila, "Atate nalakwa pamwamba pa mtambo ndi pachogolo pamaso yanu. 19Sindienela kutanidwa mwana wanuncho; nichiten ngati mmojhi wa atumiki wanu."20Ndipo wadachoka wadapita kwa atate wake. Yapo wadali wakali kwakutali atate wake adamuona adamuonela lisungu adathamanga liwilo ndi kumkumbatila ni kumbusu. 21Yujha mwana wadaakambila, atate ndalakwa pamwamba pa mtambo ndi pachogolo pa maso yanu sindienela kutanidwa mwana wanu.'22Wajha atate wadaakambila atumiki wao, jhanachoni chisanga chivalo chili cha bwino, mukamveke mvekeni ndi pindilo pa chala ndi viatu mmyendo. 23Nampho majhanayoni ndama yujha wanona mukamchinje tidye ndi kusangalala. 24Pakuti mwana wanga wadafa nayo wali wamoyo. Wadasowa nayo waonekana adayamba kuyangala.25Nampho yujha mwana wake wamkulu wadali kumunda yapo wadalin'kujha ndi kuikhalibia nyumba wadaivela sauti ya nyimbo ndi magule. 26Wadamtana mtumiki mmojhi wadamfuncha vinthu ivi mateyake chiyani? 27Mtumiki wadamkambila mpwako wafika atate wako ampela nyama kwa chifuko wabwela bwino.'28Mwana wa mkulu wadakwiya wadakana kulowa mkati ndi atate wake adatuluka kubwalo ndi kumpembeza. 29Nampho wadaayankha wadakamba, 'Penyani ine nakutumikilani vyaka vambili, nampho sinida lakwe lamulo lanu, nampho simudanipache mwana wa mbuzi, kuti ni khoze kusangalala ndi mabwenji yanga. 30Nampho yapo wafika uyu mwana wanu uyo wadawananga chuma chanu chonche pamojhi ndi mahule mwamchinchila ndama uyowanona.31Atate adamkambila, 'Mwanawanga, iwe ulipamojhi ndi ine siku zonche ndi vonche ivo nilinavo ni vako. 32Nampho idali bwino kwatu kuchita chisangalalo ndi kuyangala, uyu m'bale wako wadafa, ndi saino wali wa moyo, wadasowa nae waonekana."

Chapter 16

1Yesu wadakambilancho ophuzila, "Padali muntu mmoji fulu uyowadali ndi meneja uyowadakambidwila kuti meneji wawananga chuma chake. 2Ndichimwecho fulu uyo wadamtana wadamkambila ni chiani ichi chichivela pakati pako? Chocha.'3Yuja meneja wadakamba muntima mwake, nichite chiyani pakuti ambuye wanga anichchelamchito yanga ya umeneja? Nilibe phavu zolima nikupemba nichatamanyazi. 4Ndijiwa ichosinichite ili yaposinichochedwe panchi to yanga uwakili wantu anikalibishe mnyumba wao.5Ndi chimwecho adawatana wadeni wa ambuye wake kilammoji adamkambila udaidwa kiasi chanji ndiambuye wako?' 6Wadakamba vipimo mia moja va mafuta adamkambila tenga hati yako chitema lemba hamsini.' 7Patela adamkambila mwina ndi udaidwa mtengo wanji?' Wadakamba vipimo miamoja va ufa wangano adamkambila tenga hati yako lemba themanini.'8Yuja ambuye wadamyamika meneja dhalimu kwa ivo wadachita kwa wereu. 9Pakuti wana apajikolino. Nane nikukambila jichitileni mabwenji kwachuma cha unkhungu iliyaposi palemekeleke kukalibisheni kupitila mako ya milele.10Wali oaminika kupitila lililaling'ono sana kukale laliku lupia. 11Ngati anyiimwe simdali oamika kupitila chuma chaunkhu ngu ndi yani uyosi kuamini kupitila chuma chuma cha zene? 12Ni ngati simdali oamika katika kutumia cha muntu cha muntu mwina ndi yani siwakupacheni chanu machinawene?13Palibe mtumishi wakoza kutumia achaambuye awili pakuti siwamuipile mmoji ndi kumkonda mwina, au siwagwilane ndi uyu ndi osamlekezehu . Simkoza kumtumikia Mulungu ndi chuma."14Basi Mafarisayo, anyiyao amakonda dalamaada yavela yajayonche adamsaliti. 15Ndi wadakambila, "Anyiimwe nde mjichita haki mbele za wantu, nampho Mulungu waijiwa mitima yanu. Pakuti ilolaveka kwa wantu likalo loipa mbele za Mulungu.16Sheria ndi manabii vidalipo mpaka Yohana yapowadaja. Tangu nyengo imeneyo, bahari ya bwino ya ufalme wa Mulungu idatangazidwa ndikila muntu kuyesa kujilovya kwa mphavu. 17Nampho ndi rahisi kwa kumwamba ndi panjivichochendwe kuliko hata herufi imoji ya sheria ilemekele.18Kila wamsia mkazake ndi kumkwata mwina wazini nayo wamkwata uyo wasiidwa ndi mmunake wazini.19Padali ndi muntu mmoji fulu wadala nchalu zarangi ya zambarau ndi tai yabwino ndi wadali kusekelela kila siku ufulu wake. 20Ndi kafukanyika mmoji jina lake Lazaro wadaikidwa pageti pake, ndi wali ndivilonda. 21Nyo wadali wamukumbila kukutichidwa makomboya magwa katika meza ya yuja fulu ata agalu amaja kumnyambita vilonda vake.22Ikakala yuja kafukanyika wadafa ndi wadatengedwa ndi malaika mpaka pamtima pa Ibrahimu. Yuja fulu nayo wadafa wadazikidwa. 23Ni kuja kuzimu yapowadali katika mateso wada yainua maso yake wadamuona Ibrahimu kwa patali ndi Lazaro pamtima pake.24Wadalila wadakamba, 'Tata Ibrahimu, nichitile nilisungu mtumeni Lazaro wachovye incha yachala chake mmoji au buludishe lilime langa pakuti niteseka katika moto una.25Nampho Ibrahimu wadakamba mwnanga kumbukila kuti katika maisha yako yayowayalandila mambo yako ya bwino, ndi Lazaro chimwencho wadapata yoipa ila chipano walipo wantondozedwa ndi iwe upwetekedwa. 26Ni zaidi yayameneyo kwaikidwa jenje laukukono kupita kwanu sadakoza wala wantu akwasada yomboka kuja kwantu.'27Yuja fulu wadakamba, nikupempha ambuye Ibrahimu, kuti amtume kukomo kwa ambuye wanga. 28Pakuti nilinao abale asano ili awaonyekwama kuti iwo nao saaje paalo pamateso.'29Nampho Ibrahimu wadakamba, 'Mwana wanga Musa ndi manabii. Aiye avechele anyio. 30Yujha fulu wadakamba, palibe ambuye Ibrahimu, nampho ngati wakaendelea muntu wachokoyo kwa wafu siwatubu.' 31Nampho Ibrahimu wakambile, ngatisiwavenchela Musa ndi manabii sashawishika hata muntu wa kafufuka katika wafu.

Chapter 17

1Mpulumusi wadakambila opuzila wake, "Vinthu visababisha wanthu achite chimo, ni lazima yachokele, Nampho ole wake munthu uyo wasababisha! 2Idakakakala cha bwino ngati munthu mmeneyo wadakamangidwa mwala olemela osagila mkosi ni kutaidwa mmaji, kuliko kumchita mmoji wa anyiyawa wana achite chimo.3Jisungeni. Ngati mbale wako wakakulakwila muonye, naye wakalapa mlekelele. 4Ngati wakulakwile mara saba kwa siku limoji, ni mara saba kwa siku limoji wakuja kwako wakamba, 'nilapa,' mlekelele!"5Opuzila wake wadakqmbila Ambuye, "Mtuongezele chikulupi chatu." 6Ambuye adakamba, "Ngati mdakakala ni chiku lupi ngati punje ya haradali, mdakakoza kuukambila mtengo uu wa mkuyu, 'Zuka ni ukapuke mnyanja,' nao udakakuvelani.7Nampho yani kati yanu, uyo wali ni wakumtumikila walima munda au uyo wawesa mbelele, wamkambile pobwela kumunda, maja chisanga ni kala uje chakuja? 8Au siwamkambila, niandalie chakuja nije, nijimange lamba nimtumikile mpaka yapo sinimalize kuja ni kumwa. Baada ya pamenepo siuje ni kumwa.9Siwamumika mbowa mmeneyo kwa ndande wachita yaja wadakambidwila? 10Ata chimwecho namwe mkato chita yayo mwatumidwa kambani ife ni otumidwa sitivomelezeka. Tachita tu yaja yafumika kuchita.'11Idachokela kuti yapo wamachoka kupita ku Yerusalemu, wadapita mmalile mwa Samaria ni Galilaya. 12Yapo wadali nkulowa kukijiji chimoji, kumeneko wadapezana ni wanthu kumi adali ni ukoma adaima patali 13adachocha sauti adakamba "Yesu, Ambuye mtulekelele."14Yapo wadaona wadakambila, "Pitani mkajilangize kwa anchembe." nao yapo amapita adalama. 15Mmoji wao yapowadaona kuti walama, wadabwela kwa sauti yaikulu wamsifu Mulungu. 16Wadabula magoti mmyendo mwa Mpulumusi wadamuyamika. Iye wadali Msamaria.17Yesu wadayamkha, wadakamba, "Bwanji adalamu onche kumi? Ali kuti anyiwaja wina tisa? 18Palije ata mmoji waonekana kubwela dala kumuyamika Mulungu, ikapanda uyu mlendo?" 19Wadamkambila, "Ima ni upite zako chikulu pi chako chakulamicha."20Yapo wadafunchihidwa ni mafarisayo ufumu wa Mulungu ukuja chakanji, Yesu wadayankha ni kukamba, "Ufumu wa Mulungu osati chinthu icho chikoza kuonekana. 21Wala wanthu siakamba, 'Penya yapa!' au, 'Penya uko!' chafuko ufumu wa Mulungu uli mkati mwanu."22Yesu wadakambila opuzila wake, "Muda siufike ambapo simkumbile kuiona moja ya siku ya mwana wa Adamu, nampho simuiona. 23Siakukambileni, 'Penyani, uko! Penya, yapa! Nampho msapita kupenya wala kwachata, 24Ngati umeme wa mphambe uja umulika kumwamba kuyambila upande umomji mpaka wina. Chimwecho mwana wa Adamu wakale chimwecho katika siku lake.25Nampho poyamba sifunike kuzunjidwa katika vinthu vambili ni kukanidwa ni chizazi ichi. 26Ngati umo idali siku za Nuhu, nde umosikalile siku za mwana wa Adamu. 27Adaja, ni kumwa, adakwata ni kukwatiwa mpaka siku ija ambayo Nuhu yapo wadalowa katika safina ni gharika idaja ni kwamaliza onche.28Ndo umo idali siku za Lutu, adaja ni kumwa, amagula ni kugulicha, kulima ni adamanga. 29Nampho siku lija Lutu yapowadachoka ku Sodoma, idanya vula ya moto ni chiberiti kuchoka kumwamba ida maliza onche.30Chimwecho ndeumo ikalile siku la mwana wa Mulungu yapo walangizidwe. 31Siku limenelo, siudamwomeleza wali kudale ya nyumba wachike wakatenge vinthu vake mkati mwa nyumba. Ni siudamvomeleza wali kumunda kubwela kukomo.32Umkumbukile mkazake wa Lutu. 33Waliyonche waesa kulamicha umoyo wake siwayataye, nampho walimicha umoyo wake siwayataye, nampho waliyonche wautaye umoyo wake waulamiche.34Nikukambila, usiku umeneo kukale ni wanthu awili katika chitanda chimoji. Mmoji siwatengekwe, ni mmoji siwasiidwe. 35Kukale ni wachikazi awili atosaga vakuja pamoji, mmoji siwatengedwe ni mwina siwasiidwe."37Wakamwuliza, "Wapi, Mungu?" Akawaambia, "Pale ulipo mzoga, ndipo tai hukusanyika kwa pamoja."

Chapter 18

1Nde yapo wadakambila chifani cha namna umaifuni kila na kupempha yengo zencho, ndi siadadula khumbilo. 2Wadakamba, 'Kudali ndi olamula pakati pa jikho lina, ambaye siwama mbope Mulungu ndi kuwalemekela wanthu.3Padali ndi ofedwa di mmunake pajiji limela naye wadamwendela mala kambili, wadakamba, 'Ndi mtandile kupata malinga zidi ya mdani wanga.' 4Kwa nyengo ya itari siwadali tayari kumtandila, nampho baada ya nyenga wadakamba mumtima mwake, ingakhale ine sindi mwapa Mulungu au kumlemekeza munthu, 5nampho pakuti uyu ofedwa ndi mmunake wandi ncha uncha sindi mtandile kupata malinga yake, ili siwadancha kunileme ncha kwa kunijela nyenga kwa nyenga.6Ndoyapo Ambuye adakamba, venchela umowakambila uyu olamula. 7Bwa Mulungu naye siwapeleke malinga kwaochagulidwa wake anyiyawa amlilila usana ndi usiku? Bwa, iye siwakhala adikilila kwao? 8Ndi kukambilani kuti siwapeleke malinga kwao msanga. Nampho nyonga ya mwana wa Adamu yaposiwanche, bwa, siwapeze chisangalalo pa jikha?'9Nde wadakambila chifani ichi kwa baadhi ya wanthu anyiyawa ajiana achina wene kuti achinawene malinga ndi kuta kwa alemekela wanthu wina, 10'Wanthu awili adakwola kupita kukanisa kupempha: Mmanchi Mfarisayo ndi mwina uchonchencha sangha.11Farisayo wadaima wadapempha vinthu ivi pamwamba pake mwene, 'Mulungu, ndi kuyamikila pakuti ine osati ngati wanthu wina anyiyawo ndi ankhungu wanthu osati alene, achigarara, au ngati uyu ochanchencha sangha. 12Ndi manga mala kawili kwa juma. Ndi achacha chanchi kumi pakati pa vopata vanche nipata.'13Nampha yuncha achonchencha songho wadaima kutali, ndi siwadakhalo ata kupenya maso yake kumwamba, wadapwanya chidale chake ndi kukamba, Mulungu, ndilokolele ine mwene chima.' 14Ndikukambilani, munthu uyu wadabwela kukhama wawelongedwa malinga kulika yuncha mwina, pakuti kila waji kweza si wachichidwe, nampho kilamunthu wanchichincha siwainulidwe.'15Wanthu adampelekela wana wao akhanda, ili wakhale kuwaagusa, nampho opulila wake yape adaona yamoneyo, adakanila. 16Nampho Yesu wadaatana kwake ndi kukamba, asiyeni wana wang'ena anche kwanga, walamsidaakaniza. Ndande ufumu wa Mulungu ndi wa wanthu ngati anyiyawa. 17Uzene, ndikukambilani, munthu waliyonche siwaulandila ufumu wa Mulungu ngati mwana ndi uzene siwadowa.'18Otawalammenchi wamfuncha, wadakamba, apulisi abwina, ndichite chiyani ili nisiidwile umoyo wa muyoya?' 19Yesu wadamkambila, 'Ndande chiyani unitana wabwino? Palibo munthu uli wabwina, ila Mulungu yonka pe. 20Ulinchi wa lamulo- chigororo, usidapa, usidaba, siudakamba mntila, alemekeze atate wako ndi amayi wako. 21Yuncha atawala wadahamba, 'Vichito vimeneva vanche nda vigwila tangu ndi dali mnyamata.'22Yesu yape wadavela yameneyo wadamkambila, "Wachopekeledwa chichito chimanchi. Lazima ugulinche vinthu venche ulinava ndi waagawile osauka, nawe siukhele ndi chaikila kumwamba - nde unche , unichate.' 23Nampho opata yapo wadavela yameneyo, wadaipi dwa sana, pakuti wadali opata sana.24Nde yapa Yesu, wadamwona umowadaipidwa sana wadakamba, 'Nde umasiikhalile kulimba kwa epata kulewa pakati pa ufumu wa Mulungu! 25Pakuti ndi rahisi sana kwa ngamia kupita mkati mwa nchenche la sindano, kuliko kwa epata kulowa pakati pa ufumu wa Mulungu.'26Anyiwancha adavila yameneyo, adakamba, 'Ndi yani basi, siwakhale kulamichidwa?' 27Yesu wadanchibu, 'Vinthu sivikhalekana kwa mwanadamu kwa Mulungu vikholezekana."28Petro wadakamba, 'Sawa, ifi tasia kila chinthu ndi takuchota iwe.' 29Nde yape Yesu wadaakambila, uzene, ndikukambilani kuti palibe munthu oyowasi ya nyumba, au wamkazi, au mbale, au akumbala wake au wana, ndande ya ufumu wa Mulungu, 30ambayo siwalandila vambili zaidi pakati panchiko lino, ndi pakati pa nchika likuncha, umoyo wa muyaya.'31Baada ya kwaakusanya anyiwancha kumi ndi awili, wadaakambila, 'Penyani, tutukwela kupita ku Yerusalemu, ndi vinthu vonche ambavo valembedwa ndi ainesa kuhusu Mwana wa Adamu siyakamilishidwe. 32Pakuti si wantilidwe mmancha mwa wanthu anyi yawo siamjiwa Mulungu ndi sichitidwe mpepu ndi ncheuli, ndi kulavulidwa malovu. 33Baada ya kumtyapa viboka siamuipe ndi siku ya katatu siwa hyuke.'34Siada elewo vinthu vimenevo, ndimau limenelo lidali lobisidwa kwao, ndi siadaelewe vinthu iva vidakambidwa.35Idali Yesu yapo wakhalibia ku Yeriko, munthu mmonchi siwaponya wadakala mphepete ma barabara ndi wapempha mtandizo, 36Yapo wadavela gulu la wanthu ndilipita wadafu ncha ndi chiyani chichekela. 37Adamkambila kuti Yesu wa Nazareti wapita.38Nchimwecho yuncha osapenye wadalila kwa sauti, wadakamba, 'Yesu, Mwana wa Daudi, undilekelele.' 39Anyiwancha amaenda adamkalipila yuncha siwapenya, adamkambila ukale kachite. Nampho iye wadazidi kulila kwa sauti, 'Mwana wa Daudi, undilekelele.40Yesu wadaima wadalamula munthu yancha wapelekedwe kwake, Nde yapo yuncha osapenya wademkalibia, Yesu wadamfuncha, 41'Ufuna ndikuchitile chiyani?' Wadakamba, 'Ambuye, ndifuna ndi penye.'42Yesu wadakamba, 'Upate kupenya. Chikulupi chaka chakulamicha.' 43Nyengo imwe yo wadapata kupenya, wadamchota Yesu ndi wadamyamikila Mulungu. Yapoadaena limelelo, wanthu wanche adamsifia Mulungu.

Chapter 19

12Yesu wadalowa ndikupita katikati mwa Yeriko. Pamenepo wadalipo munthu mmoji amatana Zakayo. Lye wadali wamkulu wa osonkhecha sonkho ndi wadali opata.3Wamayesa kumuona Yesu ndi munthu wa mtundu uti, nampho siwadakhola kumuona chifukwa chagulu la wanthu, ndande wadali ofupika. 4Kwaicho, wadatamanga pachogolo pawanthu, ndi kukwela mumkuyu kuti wakhoze kumuona, chifukwa chake Yesu wadali pafupi kupita njila imeneyo.5Nyengo Yesu wadafikha malo yaja wadaphenya mmwamba ndikumkambila Zakayo, chikha msanga, pakuti lelo ndi funika kulongeza mnyumba mwako.' 6Wadachita msanga, wadachika ndikumlandila mokondwa kupunda. 7Yapo adaona izi wanthu wonche, adadandaula, ndikukamba waphita kumuyendela munthu wa machimo.'8Zakayo wadaimwa ndi kukamba Ambuye, penyani hafu ya chuma changa ndaninkha osauka ikhakala ngati ndamlanda munthu ayenche chinthu, sindimbwezele kanai.' 9Yesu wadamkambila lelo chipulumuso chafika mnyumba mwako, ndande iye naye ndi mwana wa Ibrahimu. 10Ndande mwana wa munthu wajha kufunafuna ndi kuombola wanthu adataika.'11Yapo adavela izi, wadaendekela kunena ndi kuchocha fanizo, ndande wadali pafupi ndi Kuyerusalemu, anyaio amagani za kuti ufumu wa kumwamba udali pafupi kuoneka mara kamojhi. 12Kwaicho wadakambila, mkulu mmoji wadapita kujhiko la kutali kuti wakaulandile ufumu ndi kubwela nao.13Wadaatana anchito wake khumi, ndikwaninkha magulu khumi, ndikwakambila, chitani malonda mbakana yaposindibwele.' 14Nampho wanthu wake adamuipila kwa icho adatumiza wanthu amchate ndi kumkambila, sitifuna munthu uyu wakhale mfumu wathu.' 15Idali yapo wadabwela kukomo wali mfumu, wadalamula atanidwe kwa iye, wakhoze kujhiwa pindu lanji apheza pambuyo pochita malonda.16Wadajha oyamba, wadakamba, 'Ambuye ndalama yanu ija yapindula ndalama khumi.' 17Mkhulu yuja wadamkambila, chabwino, wanchito wa bwino, ndande udali okulupilika pa chinthu cha ching'ono, siukhale ula mulila mijhi khumi.'18Wadajha wakhawili, wadakamba, 'Ambuye ndalama zako zijha zapindula makhumi asano.' 19Mkhulu yujha wadamkmambila kuti iwe siulamulile mijhi isano.'20Ndi mwina wadajha, ndi kunena, 'Ambuye iyi yapha ndalama yanu, iyo ndinda kusungila bwino pakanchalu, 21Ndande ndidaopa iwe ndi munthu okhalipa. Uchichocha icho siudachiike ndi kugoola icho siudachivyale.'22Wamkhulu yujha wadamkambila, kwa mau yako umwene, sindikhulamule, iwe wanchito oyipha, udajhiwa kuti ine ndi munthu okhalipa, nditenga icho sindidachiike ndikugoola icho sindidavyale. 23Chiphano mbona ndalama zanga siudaziike ku benki, kuti ndikhabwela ndikatenge ndi pindu?24Wamkulu yuja wadaakambila wanthu anyiao adangoimaima pamenepho, mlandeni ndalama zo ndimumninkhe uyo walindi ndalama makhumi khumi.' 25Adamkambila, 'Ambuye mmeneyo wali ndi makhumi khumi.26'Ndikukhambilani kuti uyo walinacho siwapachidwe kupunda, nampho uyo walijhe hata chochepha walinacho sichitngedwe. 27Nampho anyiawa adani wanga, sadafune ndikhale fumu yao, jhanaoni pano ndi aphedwe pamaso panga."28Wakate kukhamba yaya, wadaendekela mchogolo kukwela kupita ku Yerusalemu.29Idali yapho wadali pafupi du mujhi wa Bethfage ndi Bethania, pafuphi ndi philila mizeituni, wadatumiza omphuzira wake, 30ndikunena pitani mujhi wa pafupi. Mkalowa mkamupeza mwana wa bulu wali pachingwe, kamasuleni mujhe naye. 31Ngati munthu wakakufunchani, bwanji mu mmasula? Kambani, "Ambuye amfuna."32Anyiwajha adtumidwa adapita ndikumwona mwana wa bulu ngati Yesu umowadaakhambila. 33Yapho amammasula mwana wa buu achina wene wao afuncha ndande chiyani mummasula mwana wa bulu uyu?' 34Adakamba, amfuna Ambuye. 35Ndipo adamupelekela Yesu, adayala nchalu zao pamwamba pa mwana wa bulu ndi kumukwezapo Yesu. 36Yapo wamaphita wanthu adayala vivalo vao mnjila.37Yapho wamachikha phili la mizeituni, omphuzira wake onche adayamba kukondwerera ndi kutamanda Mulungu pakukweza mau, chifukwa cha zochita zazikhulu izo adaziona, 38ndikukamba, 'Ndiye yodalisidwa fumu iyo ikujha mjhina la Ambuye! Mtendere ku mwamba, ndi ulemelelo kumwamba mwamba!'39Afarisayo akumojhi pa msonkhano adamkhambila, aphuzisi, akhalichechete ophuzira wako.' 40Yesu wadayankha, ndi kunena, ndikukambilani, ngati akhakala chete anyiawa, miala sikweza mau.'41Yesu yapho wadausendelela mujhini wadau lilila, 42Ndikukamba ngati ukadajhiwa iwe, zinthu izo iwe zikupelekela mtendere, nampho chiphano yabisika pamaso pako.43Pakuti masiku yakujha yapho adani wako samange chisani pafupi ndi iwe, ndikukuzungulila ndi kukuchekheleza malo yonche. 44Sakugweche panchi iwe ndiwana wako, sakusiila mwala pamwamba pa mwala unjakhe, ndande siudajhiwe nyengo Mulungu yapho wamayesa kukhuombola.45Yesu wadalowa nyumba ya Mulungu, ndi kuyamba kwa thopola anyiwajha amagulicha, 46ndikwakambila, "Yalembedwa, 'Nyumba yanga sikhale nyumba ya maphemphelo, nampho anyaimwe mwaichita phanga la achifwamba."47Kwaichi Yesu wamayaluza sikhu ndi sikhu mnyumba ya Mulungu. Akhulu anchembe, ophumzisa ndi amalamulo ndi achogoleli a wanthu amafuna kumupha, 48nampho sadakhole kupheza njila yochitila chimwecho, ndande wanthu wonche adali ovechela mau yakhe.

Chapter 20

1Idali sikulimoji, Yesu yapowadali ndi waluza wandu mnyumba ya mulungu ndi kupembela ulaliki, kuwani wakulu ndi apuzisi amalamulo ada mpitila pamoji ndi azee. 2Adamzungulila, ndi akambila, ''Tukambile ndi kwamalamulo yanji uchita vindu ivi? Au yani nyo ambae wakunikha malamulo yaya?''3Naye wadayakha, wadakambila, 'Nanenjo sindikufunjeni yango. Mundi 4kambile, ubatizi wa Yohana. Bwa, udachoka kumwamba au kwawandu?'5Nambo adakambilana anyiiwo kwa nyi iwo, akakamba, ''Udachoka kumwamba, siwatufunje, 'Basi, mbona simudamwamini?' 6Ndi tukakamba; udachoka kwawandu; onje pano satutimbe myala, mana onje akulupilila kuti Yohana wadali mlosi.''7Ndipo, adamnyakha ya kuti samajiwe ukuidachoka. 8Yesu awadakambila, '''Nane ine sinikukambilani imwe ndi malamulo yaya ni nichita vindu ivi.''9Wadakambila wandu chifanizo ichi, ''Mundu mmoji wadalima munda wamzabibu, adali kodicha koolima mizabibu, na ndikupita kujiko lina pandawi yaitali. 10Pandawi idakambilidwa, nadamtuma wanjito koolima mizabibu, kuti amminge malo ya vipacho va munda wa mizabibu. Nambo alimi amizabibu adamtimba, adambwe za manja - youma.11Ndipo wadamtumanjo wanjito mwina ndi nayo adamtimba, kuchita kuupa, ndi kumbweza manja - yachomwe. 12Wadamtumanjo wakatatu ndi naye adampweteka ndi kumponya kubwalo.13Chomwe ambuye amunda adakamba, ''Sinichite chiyani? Nituma mwana wanga chikondi pena samulemekeze.' 14Nambo alimi amizabibu yapo adamuona adakambilana anyiiwo kwa nyiiwo ndakamba, ''Uyu nde mrithi. Tumpe, ili ulithi wake ukale kwatu.'15Adamchocha kubwelo kwa munda la mizabibu ndi kumpa. Bwa ambuye umunda sachite chiyani? 16Siwanje kwa apa alimi a mizabibu, ndi siwanikhe mundao wina.'' Nao yapo adavela mauyo, adakamba, 'Mulungu wakana.17Nambo Yesu wadapenya, ndi kwamba, ''Bwa malembo yo yajiwicha chiyani? 'Mwala adaukana amisili, likala mwala wapambepete?' 18Kila mundu wakangwa pamwala limenelo, siwaduke mapisi mapisi. Nambo yujasili mgwele, silindimbe.'19Hivyo alembi ndi wakudu wamabusa adafuna njila yakungwila ndawi imweyo, adajiwa kuti wakamba chifanizo ichi kuposa kwao. Nambo wamaopa wandu. 20Adampenya paubwino, adatuma kutwametume yaomajichite kuti wandu abwino, ili apeza kumpata kulakwa paulaliki wake, ili kumpeleka kwalamuli ndi iwo alamula.21Nao adamdunja, ndakamba, ''Mpuzisi, tijiwa kuti ukamba ndikuyaluza vindu vauzene ndi sindikwamiza ndi mundu mwina, nambo iwe ukamba uzene kuhusu njila ya Mulungu. 22Bwa ndiuzene kwatu kulipa msokgo kwa kaisali au noto?''23Nambo Yesu wadazindikila chifuno chao wadakambila, 24'''Nilangizeni dinali. Ngope ya picha yayani ili pamwamba [ake?'' Adakambia, '''Ya Kaisari.''25Naye adakambila, 'Basi, mnikheni kaisali yali yake kaisali, ndimulungu yali yake Mulungu.' 26Olemba ndi wakulu amabusa atalibe mbavu chokosa chija wadakamba pawandu. Adadabwa mayakho yake ndi sadakambe chilichenje.27Oche pawao amasadukayo adampitila, waja ali amakamba kuti palibe kunchidwa, 28adamfunja, amakamba, ''Mpuzishi, musawadatilembela kuti ngati mundu wa kafedwa ndi mbale wali ndiwamkazi ndi mwana basi ifunika kumtenga wa kazi wabale wake ndi kubala naye pandande ya kaka yake.29Kudali ndi mbale saba oyamba wadakwata, wadafa popande kusiya mwana, 30ndi wakawi lifo. 31Wakatatu wadamtenga vivija, chocho wa saba siwadasiye mwana ndi kufa. 32Pambuyo yuja wakazi wadafa. 33Pachogolo pozusha akufa siwakale wakazi wayani? Pakuti onje saba adali akwatila.'34Yesu wadakambila, ''Mwana ajiko lino kukwata ndi kukwatiwa. 35Nambo waja afunika kulandila kutuchidwa wa akufa ndikulowa ufulu wa mtendele sakwata wala kukwatiwa. 36Wala sokoza kufanjo, pandande kuti sawa ndaungelo ndi wana a Mulungu wana ozuchidwa.37Nambo imeneyo akufa azuchidwa, hata Musa wadalangiza pamalo katika fukutu, paja wadantana mbuye ngati Mulungu waibhahimu ndi Mulungu waislaka ndi Mulungu wa Yakobo. 38Chopano iye opande Mulungu waakufa, bali ali moyo, pandande onje akala kwake.''39Ochepa wao wapuzisi amalamulo adamuyakha, 'Mpuzisi, wayakha bwino.' 40Sadab ese kumuykha mafujo yambili kupunda.41Yesu wadakambila, ''Bwaji wandu akamba kuti Kristo ndi mwana wa Daudi? 42Mana Daudi mwene wakamba pazabuli: Ambuye adamkambila ambuye wanga; kala pajanja lakuliya, 43Mbaku ndi kuikileni oipa wako panji panywendo yako.' 44Daudi wadamtana Kristo ambuye basi sikale bwanji mwana wa Daudi?''45Wandu onje yapoadali amamvechela wadakambila opuzila wake, 46''Jioyezeni ndi olemba, olemba akonda kuenda avala viwalo vavitali, ndiakonda moni maalumu kumsika ndi mipando yaulemu katika nyumba zamulungu ndi mmalo ya ulemu ko shiliki. 47Anyiiwo njo piya akuja nyumba za afedwa, ndi kujichita asali sala zatituli. Anyi yawa salandite hukumu yaikulu kupunda.'

Chapter 21

1Yesu wadapenya wadaona waachwina alindi vachunko adanika mpaso zao moli mbikichidwe. 2Wadamwona wakazi wafedwa ndimawana wake mmoji otedwa ndiwaika ndakwozake ziwili. 3Mweno wadakamba zene ndikukambilani uyu wafecha ndinemwawake okedwa na ikazambili kupundo aunjiime anche. 4Anyiyana onche achoche panso kuchokela mvamsali amwevo nampu uyo wafedwa ndimamwene wake wachoche pakatedwa pake wachoche ndalama zonde wadelinazo chifukwe cha kulame kwake.''5Ntawi wena ndiwakamba nkani ya nyumba ya murungu imenemo idali kukonjendwa bwino ndi miale yabwino ndi vochochela wada kumba, 6''Pakati pa nkani izi muziona ntawi si kuja ziwe zisikale pauje mwala ata umoji siuusiidewe pa mwamba pa mwara umenao si ubomoledwe.''7Mmweno adamfuncha odakamba, ''Mwalimu, nkati izi sinchokaleliti? Nalinchi yani sichikale chizindikilo cha kuti nkani ize zilipafupi kuchokala?'' 8Yesu wadeyanka, ''Mkale ojipanyelelo kuti sindanyengedwa chifuko ambili siabwele kpafila jina langa ndialamba, 'Ine nde iye ndi nfawi yawandikira sinde achata. 9Mkavela nkondo ndi mavda sindoopa chifuko cha nkani izi yofunika yochakele payamba nampo potele sopachokela msanga.''10Pambuyo wade akambila, ''Jikosiliko kyambana ndi jiko liujake, ndi ulanu lilo pa ubwalilo wena. 11Sikukale ndi kutembemele kakuru ndi njali ndi nkufu malo yambili siku kale nde vichifo vo opyeza kuchokela kumwamba.12Nampo pambuyo pasachokela nkani izi zonche zialike manja yao pamwamba pani ndi kukuvutichani kukupelekani mujumba za Mulungu ndi mndande kukupelekani kwa mafume ajiko ali ndi lemulo chifukwa cha jina kuga. 13Iyi siikumasulileni vichito vabwino volangie vichifo vabwinu.14Kwaicho lamulani mmufima yanu osika chifefezo mnamsanga, 15chifykwa sindi kupancheni mau ndi vichifo vabwinu imeneyo adani ann wonche sakoza kuisiya ndi kukana.16Nampo si mkamudwe ndiobala wanu acha abale wanu apafpi namwe mabwajiranu, ndi simpedwe ochepa. 17Simuipidwe ndikira muntu chifuko cha jina langa. 18Nampo palibe chichi atawumoji la mmutu mutu silitaike. 19pakatikati pa kuvuanika kwanu simlanu cha umoyo wanu.20Yapo simuone Yerusalemu ya zungulilidwe ndi asirikuli ankondo yofunika mjiwe kuti kuwanangika kwake kulipafupa. 21Pamenepo gyowaja ali kuyudea atawile mmepili ndianyiwaja ali pakati pamnji achokepo ndi msada asia ali mmijoalowe. 22Meteyeke izi nde siku za malipilo dla kuti nkani zanche za lembedwa zikale ndi uzene.23Vudo lao acha maneo ali ndi mimba ndiache awene ayamwicha pamesika yameneyo chifko sikukale ndi mavufo yambili pakati pajoko ndi kukwiya kwa wantu sawa. 24Ndi siagwe kwa kuchogoro kwa upanga ndi siatengedwe mtenga mtenga ndi maiko yanche ndiye mesaleno si ipondedwe ndiwantu ajiko mpakana nfawi wantu ajiko siavanevavo.25Sikukale ndi chilangizilo pakati pajua mwezi ndi ntondwa ndijiko silikale ndi umpowi podwa mfima sikuchokele ndande kulila kwa mafunda yanyanja. 26Sikukale ndi want odwa mitima chifuwa cha mauta ndi chifuko chogani zila nkani sizichokela pakati pajoko chifuko pavu zamafumbo sizi vinukile.27Pambuyo pake sikwane Mwana wa Muntu ndiwachokela mmitambo pampavu za ueneleli waumulungu. 28Nampo nkani izi yapo yambe kuchikela imani kwezeni mitu yawo chifuko kulamichidwa kwanu kwa sendelela pafopa.''29Yesu adaakambila kwa chifanizi, ''Upenyeni mtengo ndi mifengo ywacho. 30Yapo ichwecho vomalela mji penyela mwa achinawene ndi kujiwe kuti mwavu ulipafupi. 31Chimoji moji yapo mwona nkani izi zi chokela onyiimwejiwani kuti ufuru wamrungu wawandikila.32Zene ndekukambilani fuko ili silipita mpakana nkani izi zonche yapo sizichokale. 33Mifambo ndi jiko si zipite nampo mau yanga siya pasilapo afapangoni.34Nampo jipenyeleleni mwachine wene dala kuti mitima yanu siida lema chadwani kumwananga kulojela ndi mavunto ya malamidwe yaya. Chifuko limenelo siku silije mwa zizizi, 35ngambi msampa chipako sikale pamwamba pa waliuenche mmweve wa kula pamaso pa jiko wache.36Nampo mkale maso ntawi zilizondwa mjipempela kuti mkale ndi mpavo kupude kukwepana ndi yaya yonche siyachokele ndi kwina pa chogoro pa mwana wa muntu.''37Mawau ntawi za usane wadali ndi wayaruzo mnyumba yamwa ndi usiku wadacho kekubwalo ndi kupita kukara kupori lifanidwa Mzeituni. 38Wafu wonche ada mjera umawa mara kumvechelo mkati mwa nyumba ya mulungu.

Chapter 22

1Ndipo sikukuu ya mkate osatilidwe kulujihka idali yawandikila, uyo imatanidwa Pasaka. 2Wakulakula aichembe ndi ohembe adapachemaghanizo ntundu wa k pha Yesu, kwa chifko adaopa wandhu.3Satani wadalowa mkati mwa Yuda Iskariote, mmojhi wa amjiwajha oponzila kumi ndi awili. 4Yuda wadapita kupachana maganizo ndi wakulakla anchembe mtundu uwo siwapeche Yesu kwa anyiiwo.5Adakondwa ndi kuvomelezena kumpacha ndalama. 6Iye wadavomela ndi kufuna malo ya kwapacha Yesu kwaanyino kutali ndi gulula wandthu.7Pasiku ya mivute yosatilidwe kulujhuka idafika, yapo mbelele ya Pasaka cha mulinga ichochadwe. 8Yesu adatume Petro ndi Yohana, ndikunena, ''Mapitani mkati konjele chakudya cha Pasaka kuti tijhe kuchidya.'' 9Adamfujha, ''Kuti ufuna tiyachile ya maneyo ya ku konjela?''10Wadeyankha, ''Vachelani, yaposimkale mwalowa mmjhini,, wamune uyo wabala nchuko wa majhi siwapezane ndi anyiimwe. Mchateni myunda iyo siwalowe. 11Ndipo mkambileni wamkul wa nyumba, ''Punzisi wakukambila chilukiti chumba cha alendo, pamalo yapo sinidye Pasaka ndi opunzila wanga?''12Siwakulangizeni chumba cha kumwamba icho chisitayari. Chitani kkonjekela mwenemo.'' 13Mmwemo wadapita, ndi kupezana kila kandhu ngati umoadakambila. Ndipo adakonja cha kudya cha Pasaka.14Nyengo yapoidafika adakala ndi anyiwajha atumiki. 15Ndipo adakambila, ''Nditi ndiliyho lalikulu ya kudya sikukuu iyi ya Pasaka ndi anyimwe kabla ya kuvtichidwa kwanga. 16Pakuti ndikukambilani, sinidya ncho mpakana yaposikwa nilizidwa pa ufumu wa Mulungu.''17Ndipo Yesu wadatenga chikombe, ndi yapowedata kuyawikila, wanena, ''Tengani ichi, ndi mgawane amyimwe kwa anyimwe. 18Kwa mate ndi kukambila, sinimwancho chobadwa cha mpelesa, mpakana ufumu wa Mulungu yaposifike.''19Ndipo adatenga mkate, ndi yapowadata ku yamikila, wadaudula, ndi kwapacha, kunena, ili ndi tupi langa ilo tachochedwa kwa chifko cha anayiimwe chitauni chimwechi kwa chikumbukumbu cha ine.'' 20Adatenda chikombe chi mwechojhe pawo uyo pa chakudya cha usiku kunena, ''Chikombe ichi ndi mavomelezano ya chipano pa mwazi wanga, wo udamwamzika kwa chifko cha anyiimwe.21Nampho penyani. Yjha wamelonde woli pamojhi ndi ine pameza. 22Kwamate mwana wa Adamu kwa zene wapite kwake ngati uwoideto lamulidwa nampho chonde kwa mundhu yujhi uyokupitila iye Mwana wa Adamu wachidwa malonde!'' 23Adayambe kufunchana amujiiwe kwa anyijiwo yani uwaanjiwo uyo wadaka chila chindhu chimenecho.24Ndipo yadachokela machuuchano pakatikati pawo kuti ni yani uyo wakanizili edwa kuti wakulu kuliko wanche. 25Adakambila, ''Ufumu wa wandh wa jhiko alindi ukulu pamwa ndi pao, ndi anyiwajha ali ndi malamulo pamwamba pao atanidwa olemekezeka ni achangoleli.26Nampho sifunika nditu kuti ivi kwa anyimwe. Pambunyo pake, siyani yujha wali wamkulu pakati panu wakale ngati wamngono. 27Ndi yujha wali wamate kupuda wakole ngati kapolo. Kwa ndande yti wamkulu, yujha wakala pa meza kapena yuja wakala kapolo? Bwanyi osati yujha wakala pameza? Ndi jne nikati pakati panu ngati otumikila.28Nmapho anyimwe ndiwo kwawelekela kukala ndiine pa mayeso yanga. 29Ndikupachani anyimwe ufumu, ngati mujha atate uwoodawipachile jne ufumu, 30kuti mpeze kudya ndi kumwa pameza yanga pa ufumu wanga. Ndi si mkale pa mipando ya enzi ndi mwalamutila mitundu kumi na mbili ya Israel.31Simioni, Simioni, jhiwa kuti satana wapembha akupezeni kuti akupeteni ngati ngano. 32Nampho nakupembhelasi, kuti chikulupi chake chisidya lemekele pambuyo pa kubwelancho, aimilile achabale wako.''33Petro adakambila, ''Atata, ndilitayi kupita ndi iwe midende ndi mpakana pa nyifa.'' 34Yesu wadayakha, ''Nikukambila Petro, Tambala siwadelile lelo, pakytamba, ''Siudanikamwe mara katatu kuti unijhiwa.''35Ndipo Yesu adakambila, ''Yapondida wapeleka anyimwe popande tumba mseche wa vakudya, popande vilato, kwanji mdachepedwa ndi chindhu?'' Adayankha ''Popande.'' 36Ndipo adamkambila, ''Nampho chipano, watiyenche wali nditumba, autenga pamojhi ndi mseche wa vyakudya. Yujha wadali walije upanga wafunidwa wakutiche joho lake wagule mmojhi.37Chifuko ndi kukambilani, yonche yayo yalembedwe kwa ndande yaine nditu siyakwanile, 'Ndi adatenge dwa ngati kundhu uyo wawananga tauko, chifuko chijha chidalosedwa kwa ndande yaine yakwanilichidwa.'' 38Ndipo adanena, ''Ambuye penyani! Yano pano maupanga yawili.'' Adakambila ikwana.''39Pambuyo pa chakudya cha usiku, Yesu adachoka, ngati uyo wadali kuchita nyengo ndi nyengo, wadapita kupili kwa Mzeituni, ndi opunzila adamchata. 40Yapo adafika, adakambila, 'Pemphani kuti msadalowa mmanyeso.''41Adapita kutali ndi anyiiwo ngati oponya mwala, adagwada maombono kupembha, 42ndianena, ''Atate, ngati fna nacho chelani chikombe ichi. Nampho osati ngati uwaonifunila ine naupho chikondi chako chidutidwe.''43Ndipo angelo kuchoka kumwambe adamchokela, kmtila mphemvu. 44Wali mkudwala, wadambha kwa chichimichimi kupunda, ndi chitukta chake chidali ngati midondho yakula kulu ya mwazi ndi yatondhokela panchi.45Nyengo yapowadauka kuchoka pa mapembhelo yake adajha kwa opumbila, ndi kwapeza agone kwa chifko cha chisoni chao, 46ndiadafuncha, ''Kwa ndande chiyani mgone? kani mpambhe, kuti msadalowa mmayaso.''47Nyengo yapowadeli wakati kunena, penya, gulu lalikuku la wandhu lidachokela, ndi Yuda mwijhi wa atumiki kumi ndi awili ndiwa chogoza. Wadajha pafupi ndi kuti wa mpudu, 48nampho Yesu wadamkambila, Yuda, bwanji umgulicha mwan wa Adamu kwa busu?''49Nyango wajha adali pafupi ndi Yesu yapoadapeuya yongo yachokela, adanena, 'Ambuye, bwanji tatimbe kwa upanga?'' 50Ndipo mmojhi wa anyiiwo wadammenye wajhito wa mkulu lake la kwene. 51Yesu wadanena, ''Iyi ikwana. Ndi wadagusa kutu lake, wadamlamicha.52Yesu wadanena kwa wa mkulu wa nchembe ndi kwa wakuluklu wa hekalu, ndi kwa wazwee yawo adajha ndi magawizo yena. Bwanji mwajhi ngati kuti mwajha knyombola na ndi aolanda ndi vibonga ndi mau panga? 53Yapo nidali pamojhi ndi amyiimwe siku zonche muhekalu sindaike manja yanu kumwamba kwanga. Nampho iyi ndi ntawi yako, ndi malamulo ya ndima.''54Adamgwila, adamchogoza, adampeleka kunymba ya wamklu wa nchembe. Nampho Petro wadanchetilila kwa kutali. 55Pambuyo pakati atosogha moto pa ujhu uwanda wa mkati ndi yapo adamaliza kukala panchi pamojhi, Petro wadakala pakatikati pawo.56Mtumiki mmojhi wa mkazi wadamwona Petro yapowadali wakala pa dangalila machokana ndi moto, adampenya adamkambila, ''Uyu mundhu naye wadali pamojhi ndiiye.'' 57Nampho Petro wadakana, kunena, ''Wamkazi, jne sinimjhiwa.'' 58Pambuyo pa nthawi pangono, mundhu mwina wadamwona wadanena ''Iwe nawe ndi mmojhi waamujiiwo.'' Nampho Petro wadayankha, ''Wamuna, jne otatiiye.''59Pambuyo pa ngati saa mojha chimwechi, wamuna mmojhi wada uyu mundhu naye wadali pammojhi ndi iye, chifuko ndi Mgalilaya.'' 60Nampho Petro wadanena, ''Wamuna, sinijhiwa ilounena, ''Ndipo yapo uyengo wamakambe, tambala wadalila.61Wadanganamuka Ambya adampenya Petro. Ndi Petro wadali kumbukila mau la ambuye paijha adamkambila, ''Kabla ya tambala kulila lelo, siunikane jne mara katatu.'' 62Wadapita kbwalo, Petro wadalila kwa mapwetekechedwe yochuluka.63Ndipo anyiwaja wachimuna yawoadali kumpenyelela Yesu, odampepula ndi kummenya. 64Pambuyo pa kumchicha maso, adamfuncha, kunena, ''Losa! Ndi yani wakbula?'' 65Adacheza yena yambili. Yakumzungulila Yesu ndi kumpepela iye.66Ndi ypo idali umawa wazee wa wandhu adakomamkana pamojhi wakylakul anchembe ndi olemba. Adampeleka k Baraza, 67ndianena, 'Ngati iwe ndi Kristo, tikambile, ''Nampho iye asakambila, ''Ngati nikakkambilani, simuniklupalila, 68ndingati nikakufunchani si muniyankha.''69Nampho kyambila, chipano ndi kuyendekela, Mwana wa Adam si wakale wakala kujhanja la kwene. La mphamvu za Mulungu.'' 70Wonche adanena, ''Kwa icho iwe ndi mwana wa Muulungu?'' Yesu adakambila, ''Amjimwe mwanena jne ndiye.'' 71Adanena, ''Kwa ndande chiyani tikasi kufunancho umboni? Chifko ife tachinawefe tavela kuchoka lk kamwa kwake mwene.''

Chapter 23

1Msonkhano onche udaima, adampeleka Yesu pachogolo pa Pilato. 2Adayamba kumchocholela kuti tampeza mumthuyu ndi waanganamla wanth ajiko tatu kuti palije kuchocha sonkho kwa Kaisari, ndi wakamba iye mwene ndi Kristo, Mfumu.''3Pilato wadamfunche, bwa iwe nde mfumu wa ayuda?'' Ndi Yesu wadamyankha, ''Iwe wakamba chimwecho.'' 4Pilato wadamkambila wamkulu wa nchembe ndi msonkhano, ''Siniona kulakwa kwa muthuuyu.'' 5Nampho anyiiwo adachimikiza ndi kukamba, wakunjizana wanthu, wayaluza mu yuda yonche, kuyambila kugalilaya ndi chapano wali pano.''6Pilato yapo wadavela zimenezi wadafundichila ngati munthuyu wa kugalilaya? 7Yapo wadajiwa wali panchi pa ufum wa Herode, wadampeleka Yesu kwa Herode, wadali ku Yerusalemu ma siku ya meneyo.8Herode yapo wadamuona Yesu, wadakondwa kupunda, ndande siku za mbili wadakumbila kumuona, wadavela ni vichitidwa ndi iye. 9Herode wadamnfucha Yesu kwa ma yambili, nampho Yesu siwadamuyankha chilichoncha. 10Wakuhiakulu anchembe ndi olemba adaimba ko kwiandi kumuimba mlandu.11Herode ndi asirikali wake, adamtukwa na ndi kumchita chipongwe, ndi kumveka vovalavabwino, ndi kumbweza Yesu kwa Pilato. 12Herode ndi Pilato adali mabwenji kuyambila siku limenelo (pambuyo pake adali adami).13Pilato wadaatana pamoji wa akulu anchembe ndi oimilila magulu ya wanthu, 14Wadaakambila, ''Mwanipelekela munthuyu ngati munthu uyo wachogoza wanthu kuchita voipa, penya ni yapo namfumcha pamaso panu, sinidaone kula kwa munthu uyu kukuza vonche ivo mwamuimbila mlandu anyiimwe.15Palibe, Herode wambweza kwathu, ndi penyani palibe chilichonche chienela kumlanga kufa. 16Kwaicho sinilamula watyapidwe ndi sinimsiilile. 17(Chipano Pilato wafunika kumsiilila omangidwa mmoji kwa ayuda nthawi ya sikukuu).18Nampho onche adapokosela kwa pamoji ndi kukamba mchoche mmeneyo, mmasulile Baraba!'' 19Baraba wadali munthu wadaikidwa mndende chifukwa cha kupa.20Pilato wadaakambilancho, ndi wakumbila kumsulila Yesu. 21Nampho amjiiwo adabula mapokosa ndi akamba, mumwamba pamtande, mwambe pamtanda.'' 22Wadaafncha kwa katatu, walakwa chiyani, siniona icho walakwa, kwa icho sinimtyapendi kmsiilila.23Nampho adapunda kumchimikiza, kufuma kuti Yesu wapedwe, potela kukamba kwa kudapambana. 24Kwa icho Pilato wadalamula kupacha icho amafuna. 25Wadamsilila yuja amamfna wadamanyidwa chifukwa kupa, wadamchocha Yesu umo adafunila.26Yapo amampeleka, adamgwile munthu mmoji watanidwa Simoni Wakrene, wamachokala kumunda, adamsencha mtanda ja mmbuyo mwa Yesu.27guru lalikulu la wanthu ndi wachikazi yao adali ndi chisoni ndi kudandaula chifukwa cha iye amamchata. 28Nampho wadaanganamukila, Yesu wadaakambila, anamwali aku Yerusalemu, musanililila ine, nampho jililileni mwachinawene ndi wana wanu.29Penyani, siiye nyengo yapo saakambe, adalisidwa alindi mbende ndi mimba zosabala ndi mawele yayo siyadayamwiche. 30Nde yapo saayambe kiyakambila mapili tigweleni. 31Ndande ngati achita vinthu ivi mu mtengo wauwisi sii kale bwanji mu mtengo ouma?''32Wachimuna wina awili akupha adapelekedwa pamoji ndi iye kuti apedwe.33Yapo adafika pamalo patanidwa golgotha adamuwamba pamtanda pamoji ndi akupao mmoji kwene ndi mwina kumanjele. 34Yesu wadakamba, atale akululkileni, ndande saajiwa icho achita, nao adavotera kugawana ochal zake.35Wanthu adaima ndi kupenya oimilila adamchitila chiwembu, ndi akamba, wadaapulmcha wina chipano wajiplumche mwene ngati iye ndi Kristo osankhidwa ndi Mulungu.''36Asirikali nao adampepla, adamsendelela iye ndi kumpacha siki, 37ndi akamba ngati iwe ndi mfumu wa ayuda jipulumuche umwene'' 38Kudali ndi chizi ndikilo pamwamba chidale mbedwa ''UYU NDE MFUMU WA AYUDA.''39Mmoji wa akupa waja adawambidwa wadamtukwana, ndi wakamba, ''Iwe asati Kristo? Jipulumuche umwene ndi ife'' 40Nampho mwina, wadamuyankha ndi kumchinula ndi wakamba, bwanji iwe simuopa Mulungu, nawe uli ndi lamulo limwelo? 41Ife tilipano m malinja, ndande ife tilandila icho chienela pavichito vanthu, nampho choipa.''42Ndi wadaonjezela, ''Yesu, aunikumbukile yapo siulowe mu ufumu wako.'' 43Yesu wadamkambila, '''Kulupilila nikukambila lalo lilino sikale pamoji ndiine k paradiso.''44Pamene idali nthawi ya mma 6 usama, mdima udaja pa jiko lonche mbaka mma 9 usana, 45Dangalita la jwa lidatima, nchaluyocheka pakomo pa hekal lidangambika pakati.46Wadalila kwa mphavu Yesu wadakamba, ''Atate mmanja mwanu niuka mzamu wanga, yapo wadato kamba yameneyo wadafa. 47Yapo wamkulu wa asirikali yapo wadaona yayo yadachitika wadamkuzika Mulungu ndi wakamba, zoona munthuyu wadali wamalinga.''48Nyengo gr la wanthu yao adaja pamoji yapo adaona ivo vidachitika, adabwela ndi ajibula mmatupi. 49Nampho mabwenji yake ndi achikazi yao adamchata mchokela ku Galilaya, adaima kwa kwa kutali ndi kupenya vithuvo.50Penya, padali ndi munthu watanidwa Yusufu, munthu wa bwino ndi wamalinga, 51(wadali siwadavomelezane ndi lamulo ndi vichito vao), kuchoka Armathaya, muji wa ayuda, umalindila ufuma wa Mulngu.52Munthuyu, wadamuwandikila Pilato, wadapempha wapachidwe tupi la Yesu. 53Wadamchicha, ndi kvilingila sanda, ndi kumuika mmanda idasepedwa mmwala, ndi palibe uyo wadaikidwa mandayo.54Idali siku lokonja ndi Sabato idawandikila. 55Waachikazi yao adajanao kuchokela ku Galilaya, adamchatandi adaona manda ndi tupi lake umo aligonekela. 56Adabwela ndi kuyamba kutenga mafuta yonu nkhila, sik la Sabato adapumulilangati umo lili tauko.

Chapter 24

1Chisanga kupunda siku la kuyamba la jhuma, adajha pa mainja, adapeleka. 2Adaukomana mwala waghunkhulichidwa kutali ndi mainjila. 3Adaloa nkati nampho sadalipheze thupi la ambuye Yesu.4Idachokela kuti, nyengo adachanganyikiwa kkhuza ili nyengo imweyo, wanthu awili adaima pakati pao, adavala nchal zowala. 5Wachikazi adajhala mantha ndi kukwatamicha nkhope zao panchi, wadaakambila wachikazi, ''Ndande yanji mumfunafu na wamoyo pakati pa akufa?6Palibepo pana, nampho wahyuka! Kumbukilani umowadakambana namwe wakali ku Galilaya, 7wadakamba kuti mwana wa Adamu lazima wachhochhedwe mmanja mwa wanthu amachimo ndi wasulubishidwe, ndi siku la katatu, wahyukencho.''8Anyiwajha wachikazi adakumbukila mau yake, 9ndi adabwela kuchokela kumainja ndi kwakambila nkhani ii yanche anyiwajha kumi ndi ni mmojhi ndi onche. 10Nampho Maria Magdalena, Joana, Maria make wa Yakobo ndi wachikazi wina pamojhi nao adachhochha nkhani ii kwa olosa.11Nampho unthenga u udaonekana ngati nami kwa olosa, nampho siwadaavomela anyiwajha wachikazi. 12Atanchimwecho Petulo wadauka, ndi wadathamanga kupita kumanda, ndi wadazzumila ndi kupenya mkati, wadaima sanda yokha. Petulo wadachoka wadapita kukhomo kwake wadazizwa chiani icho chachokela.13Ndi penya, awili pakatipao, amapita siku limwelo pakati pa mjhi mojhi utanidwa Emmau, uo udali maili sitini kchoka ku Yerusalemu. 14Adakambana anyaiwo kwa nyaiwo kukhuza nkhani yonche iyo idachokela.15Idachokela kuti, nyengo iyoamakambana ndi kufunchana mafuncho, Yesu wadasendela pafpi ndi kugwilizana nao. 16Nampo maso yao yadachekelezedwa pakati pa kmjiwa iye.17Yesu wadaakambila, ''Chiyani icho muchikambilila anyaimwe mwa awili nyengo nimuenda?'' Adaima pajha adaonekana ndi chisoni. 18Munthu mmojhi, jhina lake Cleopa, wadayankha, ''Bwa iwe ni munthu wa pameka pano pa Yersalemu uyo siwajhiwa vinthu ivo vichokela kumeneko siku izi?''19Yesu wadakamba, ''Vinthu vanji?'' Adamunyankha vinthu kukhza Yesu Mnazareti, uyo wadali olosa, okoza pakati pa vichito ndi ma pachogolo pa Mulungu ndi wanthu onche. 20Ndi kwaumo ali waklu amakuhani ndi ochongoza wanthu yapo adamchocha kulamulidwa nyifa ndi.21nampho tidaamini kuti iye siwauike ufulu pa israeli .etu patali ndi yaya yonche,chipano ni siku lakatatu kuyambila vintu ivi vichole.22Nampho wina wake wa achikazi adachoka pakati pa gulu lathu adatizizwicha, pamalo pokalapo pamainja umawa mawa. 23Yapo adalilepela thupi lake, adajha, adaona nampho ndoto ya angelo adakamba kutu wali wamoyo. 24Wina wake wa waachimuna anyiyao adali pamojhi nafe adapita pamainja, indi kupeza ni ngati mujha wachikazi adakambila. Nampho sadamuone iye.''25Yesu wadaakambila, ''Anyaimwe wanthu vilekwandi muli ndi mitima yolemela kamini vonche ivo olosa akamba! 26Bwa siidali lazima Yesu kuvutika kwa vinthu ivi, ndi klowa pakati pa ufum wake?'' 27Ndipo kuyambila kuchokela kwa Musa ndi olosa onche, Yesu wadakaambila vintu ivo vimkhuza iye pakati pa malembo yonche.28Yapo adausendelela jha mujhi, kumeneko uko amapita, Yesu wadachita ngati waendekela mchogolo. 29Nampho adamlazimisha, adakamba, ''Khala pamojhi ndi ife, ndande kupita ujhhulo ndi siku ngati likutha.'' Chimwecho Yesu wadalowa kupitha kkhala nao.30Idachokela kuti, nyengo wakhala nao kudya, wadatenga mkate, wadaupacha mwauwi, ndi kuudula wadaapacha. 31Ndipo maso yao yadamaslidwa, adamjhiwa ndi wadasowa gafla pachogolo pa maso yao. 32Adakambichana anyaio kwa anyaio, ''Kodi mitima yathu siidawale mkati mwathu, nyengo wamakambana nafe mnjila, nyengo wadatimasulila malembo?''33Adaima nyengo imweijha, ndi kubwela ku Yerusalemu wadaapeza anyiwajha kumi ndi mmojhi, ndi anyiwajha adali pamojhi nao. 34adakamba, ''Ambuye ahjuka zene zene, ndi amtlukila Simoni.'' 35Chimwecho wadaakambila vinthu ivo vachokela mnjila ndi mo Yesu anyaio pakati pa kuudla mkate.36Nyengo naakambilila vinthu ivi, Yesu mwene wadaima pakatikati pao, ndi kwaambila, ''Mtendele ukale kwanu.'' 37Nampo adaopa ndi kujhalidwa ndi mantha indi adaganiza kuti adauna mzimu.38Yesu wadakambila, ndande yanji mudandaula? Ndande yanji mfuncho yakwela mmitima mwanu? 39Penyani manja yanga ndi myendo yanga, kuti ine namwene. Niguseni ndi muone, kwa ndande mzimu ulibe nyama wala vifpa, ngati umo munionela ine kukhala navo.'' 40Yapowadathokamba chimwecho, wadaalangiza manja yake ndi myendo yake.41Yapo adali akati ndi chisangalalo icho chidasingizikana ndi usavomela ndi kziwa, Yesu wadaakambila, ''Bwa mli ndi chinthu chalichonche cha kudya?'' 42Adampacha chipande cha nchomba icho chidaochedwa. 43Yesu wadachitenga, ndi kuchidya pamaso pao.44Wadakaambila, ''Yaponidali namwe nidakukambila ni kuti yanche yayo yalembedwa kulamulo la Musa ndi olosa ndi Zaburi lazima yaenele.''45Ndipo wadamasula njelu zao, kuti akhoze kyagwila malembo. 46Wadaakambila, ''Kti yalembedwa, Kristo lazima waznjike, ndi kuhyukancho kuchokela pakati pa akufa siku lakatatu. 47Ndi toba ndi kulekelela kwa machimo lazima ikambililidwe kwa jhina lake kwa maiko yonche, kyambila kuchoka ku Yerusalemu.48Anyaimwe ni amboni a vinthu ivi. 49Penyani, nikupelekelani ahadi atatewanga pamwamba pan. Nampo lindililani yapa pamujhi, mbakana yapo simuvekedwe mphav kuchokela kumwamba.50Ndipo Yesu wadaachongoza kubwalo mbakana yapo adali pafupi ku Bethania. Wadayanyakula manja yake kumwamba, ndi kwaapacha mwawi. 51Idachokela kuti nyengo wamaapacha mwawi, wadasia ndi kutengedwa kumwamba.52Basi adamlambila, indi kubwela ku Yerusalemu kwa chisangalalo cha chikulu. 53Adandekela kukhapo muhekalu, na ampacha mwawi Mulungu.

John

Chapter 1

1Kale lidalipo mau ndi mau lidali pamoji nde Mulungu ndi mau wadali Mulungu. 2Uyu mau kale wadali palimoji ndi Mulungu. 3Vinthu vonchi vidachitika kupitila iye ndi palibe iye palibe hata chinthu chimoji ichochidali chachitika.4Mkati mwake mdali umoyo, ndi umene umoyo udali dangalila la wantu onche. 5Dangalila lidamulika kumdima wala mdima siudatimike.6Padali ndi muntu uyu wadatumidwa kuchokela kwa Mulungu iyo jina lake wadi Yohana. 7Wadaja ngati shahidi kushuhududi kuhusu lija dangalila kuti onche akoze kuamini kupitila iye. 8Yohana siwadali dangalila lakweli ambayo washuhudie kuhusu lija dangalila.9Limenelo lidali dangalila lakwele ambayo idali imoja kupitila jiko lao kumtila dangalila kila mmoji.10Wadali katika jiko ndi jiko lidakonjedwa kupitila iye ndi jiko silimdajiwe. 11Wadaja kwa vinthu vake, ndi kwa wanthu wake sii amlandile.12Ila kwa anyiwaja ambili yao adamlandila amba adaliamini jina lake kwa anyiao adapacha malinga yakukala wana Amulungu. 13Ambao adabadwa, osati kwa mwazi wala kwa chikondi cha awili wala kwa chikondi cho munthu ila kwa Mulungu mwene.14Nalo mau lidachitika tupi ndi adalama mmitima mwatu, tawona ulemelo wake ulemelo ngati wamunthu yoka wapayoka uyo wadaga kuchokela kwa Ambuye wajala chimwemwe ndi kweli. 15Yohana wadamshuhudia kuhusu iye ndi wakukweza sauti wadakamba, "uyu ndiye ambaye nidakamba nkhani zake nidakaka yuja siwaje pambuyo panga ndi wamkulukwiko ine kwa kifuko wakala kabla yanga."16Pakuti kuchokela kupitila kukamilika kwake ife tanche talandila bure kipawa pambuyo cha kipawa. 17Pakuti lamulo lidapelekedwa kupitila Musa chimwemwe yaliyonche, muntu yote ambaye Mulungu wali katika chifua cha mbuye Yesu Kristo. 18Palibe mwanadamu uyu wamuona Mulungu nyango yaliyonche yoka ambae ndi Mulungu wali katika chifua cha Ambuye amdita iye wajiwike.19Ni uunde ushuhuda ya Yohana nyengo makuhani ndimala mi adatumidwa kwake ndi Wayahudi kumfuncha, "iwe ndi yani?" 20Bila kusitasita ndi siwadakane, ila wadayankha, ine osati Kristo. 21Ila adamkambilka, "iwe ndiyani, ili kuti nikupache niyankho ilo atituma?" Jishuhudie iwe mwene.22Kwa chimwecho adamfuncha, kwaiyo iwendi yani? Chipano. Iwendi Eliya wadakamba ine osati. 23Adakamba, iwe ndi nabii? wadayankha osati. Wadakamba, "inendi sauti yake walita kunyikani"24Nampho kudali ndi wanthu atumidwa paja kuchoka kwa Mafarisayo. Adamfuncha ndi kukamba, 25"ndande yanji ubatiza basi ngati iwe osati Mkristo wa Eliya wala nabii?"26Yohana wadayankha wadakamba nibatiza kwa maji ata chimwecho pakati panu waima munthu uyu simusiwa. 27Uyu nda uyo wadaja pambuyu paunga! Ine sinistahili lulegeza chingwe va viatu vake. 28Vinthu ivi vidachichika kume Kubethania, kung'ambo ya Yordani pamalo ambapo Yohana wamabatiza.29Siku lidachata Yohana wadamuona Yesu niwaja kwa kurake penya mwana mbelele wa Mulungu waitenga dhambi ya pajiko. 30Uyu ndo uyo wakamba nkhani zake nikakamba, "uyu siwaje kumbuyo kwanga ndi wamukuru kuliko ine pakuti wadali kabla yanga. 31Sinidamjiwe iye nampho idachitika chimwecho ili kuti wavunukulidwa Israeli, kuti nidaja nidabiza kwamaji."32Yohana wadashuhudia wadaopna roho niichika kuchoka kumwamba mfano wa dau nchi ikakala kumwamba kwake. 33Ine sinidamjiwe nampho iye wadaitumaini nibatize kwa maji wadanikambila, "yuja ambayo swane Roho Mtakatifu. 34Naona ndi nashuhudia kuti uyu ndi mwana wa Mulungu."35Tena siku litachata Yohana wadali waima pamoji ndi opuzila wake awili. 36Adamuona Yesu niwaenda ndi Yohana wadakamba "penye mwana wambelele wa Mulungu."37Opuzila awili adamvela Yohana wamakamba adamchata Yesu. 38Tena Yesu wadang'anamuka ndi kuwaona opuzila waja namchata adamkambila mfuna chiani yankha, "Rabbi, (chifuko chake apuzisi alamakuti?)" 39Adamkambila, majani ndi muone potela adapita ndi kupaona pamalo ayapo wadali wamalama, adakala pamoji nae siku limene pakuti idali yapata ngati saa kumi chimwe.40Mmoji wanyiwaja awili anyioadamvela Yohana ni wakamba nipotela kumcha Yesu wadali ndi Andrea mbale wake Simoni Petro. 41Wadamuona m'bale wake Simoni ndi kumkambila tampacha masihi (ambayo itafasili Kristo). 42Adampeleka kwa Yesu wadampenya ndi kukamba iwe ndi Simoni mwana wa Yohana siutanidwe Kefa, (naana yake Petro).43Siku lidachata nyengo Yesu yapowadafuna kuchoka kuchita Kugallaya wadampata Filipo ndi kumkambila, "nichate ine." 44Filipo wadali mwenyeji wa Bethasaida jiko laandiandi Petro. 45Filipo wadampata Nathanaeli ndikumkambila jampata yuja ambayo Musa wadalemba nkhani zake kupitila sheria za wanabii Yesu mwana wa Yusufu kuchoka Kunazareti.46Nathanieli adamkambila "bwanchitucha bwino chikoza kuchokela Kunazarete?" Filipo wadamkambila maja ndi unione. 47Yesu wadamuona Nathanieli niwaja kwake ndi kukamba "penya Mwisraeli kweli kwakweli osati wamtila mkati mwake!" 48Nathanieli wadamkambila, "wanijiwa bwanji ine"? "Yesu wadayankha ndi wadanikambila Filipo siwadakutane yapo udali panchi pamtengo ndidakukambila."49Nathanieli wadayankha, "Rabbi, iwe umona wa Mulungu! Ndi Mflume wa Israeli!" 50Yesu wadajibu wadamkambila chifuko nidakukambila nidakuona panchi pamtengo bwa wamini siwaone vichicho vavikwa kuliko ivi. 51Yesu wadakukambila, "Amini Amini, nikukambilani sizione mbingu nizichakuka ndi kumwona malaika wa kweli ndi kuchika pamwamba pa mwana wa Adamu."

Chapter 2

1Baada ya siku zitatu, kudali ni ukwati kuja ku Kana ya Galilaya ni mama wake Ampulumusi adali kumweko. 2Mpulumusi ni opuzila wake adali alalikidwa katika ukwati.3Muda atedwa ni mvinyo, mama wake Mpulumusi adamkambila, "alije divai." 4Mpulumusi wadayankha, "wamkazi imeneyo inihusu chiani ine? Muda wanga ine ukali udafikile." 5Mama wake wadakambila otumikila, "chalichonche icho wakukambileni chitani."6Basi kudali ni michuko sita ya myaka paja idaikidwa kwa chifuko cho samba katika sikukuu za Wayahudi, kila limoji lidali ni ujazo wa nzio ziwili zitatu. 7Mpulumusi wadakambila, "vijazeni maji michuko ya myala," adajaza mpaka pamwamba. 8Baadae wadakambila otumikila, "tengani pang'ono saino mpeleke kwa uyo watumikila wamkulu wa meza!" Adachita ngati umo wadakambila.9Otumikila wamkulu wadalawa yaja maji yadali yang'anamuka ni kuka3la divai, ila siwadajiwe uko yachoka (nampho otumikila atunga maji adajiwa uko yachoka). 10Kumkambila, "kila mmoji wayamba kwapacha wanthu divai ili ya bbbbb ni akatolewa wapacha divai ili yoipa. Nampho iwe waitunza divai ili yabwino mpaka saino."11Yodabicha yaya ya Kukana ya Kugalilaya, idali nde Kuyamba kwa malangizo ya vodabicha wadaita Mpulumusi, wamavunukula ufulu wake, chimwecho opuzila wake adamkulupalila.12Baada ya ili, Mpulumusi mama wake, abale wake ni opuzila wake adapita katika muji wa Kapernaumu ni adakala kumeneko kwa siku zochela.13Basi Pasaka ya Wayahudi idali yawandikila, chimwecho Mpulumusi wadapita Kuyerusalemu. 14Wadapeza ogulicha ng'ombe, mbelele, ni nkhunda, mkati mwa nyumba ya ibada. Pia niobadilisha ndalama adali akala mkati mwa nyumba ya mapemphelo.15Mpulumusi wadakonje chiboko uli ni vifundo, wadachocha onche adali mnyumba ya mapemphelo ikakalamo ng'ombe ni mbelele. Wadamwaza ndalama za obadili ndalama ni kuzivunukula meza zao. 16Kwa ogulicha nkhunda wadakambila, "chochani vinthu ivi patali ni malo yano, siani kuichita nyumba ya atata wanga kukala pamalo pa msika."17Opuzila wake adakumbukila kuti idali yalembedwa, "nchanje ya nyumba yako siinije." 18Wakulu akulu Akuuyahudi adayankha, adamkambila, "ni langizo lili ilo ulilangize kwa ndande uchita mambo yaya?" 19Mpulumusi wadayankha, "ibomoleni nyumba ya mapemphelo ii nane nane siniimange baada ya siku zitatu."20Nampho wakuluakulu Ayuyahudi adakamba, "idatenga vyaka arobaini na sita kumanga nyumba ii ya mapemphelo ii nawe ukamba uimange siku zitatu?" 21Ata ngati, iye wadakamba nyumba ya mapemphelo wanamaanisha tupi lake. 22Chimwecho pambuyo baada kuhyuka kwake kuchoka kwa akufa, opuzila wake adakumbukila kuti wadakamba chimwecho, adakulupalila malembo ni mkambo uu ambao Mpulumi wadali watoukamba.23Yapo wadali Kuyerusalemu wakati wa Pasaka, nthawi ya sikukuu ambili adakulupalila jina lake yapo adaona langizo la vodabwicha. 24Nampho Mpulumusi siwadali ni chikulupi nao kwa ndande wadajiwa wanthu onche. 25Siwadafune munthu waliyonche kumkambila kuhusu umoali wanthu kwa ndande wadajiwa icho chili mkati mwao.

Chapter 3

1Basi kudali ndi Farisayo ambayo jina lake Nikodemu mmonchi wa otumidwa pakati pa bwalo la Wayahudi. 2Munthu uyu, wadamchata mbuye Yesu usiku ndi kumkambila, "apuzisi, tujiwa kuti uli puzisi, kuchoka kwa Mulungu, pakuti palibe munthu wakhoza kuchita viwalilo ivi vonche Mulungu siwadakhala pamonchi naye."3Yesu wadanchibu, "uzene, uzene, munthu siwakhoza kulowa pakati pa ufumu wa Mulungu ngati siwabadwa mala ya kawili." 4Nikodemo wadakamba, "munthu wakhoza kubadwa wali mdala? Siwakhoza kulowa mmimba mwa mama ake mala ya kawili ndi kubadwa, bwa wakhoza?"5Yesu wadanchibu, "uzene, uzene, munthu uyo siwabadwa kwa maji ndi mzimu, siwakhoza kulowa pakati pa ufumu wa Mulungu." 6Icho chabadwa kwa nthupi ndi nthupi, ndi icho chabadwa kwa Mzimu ndi mzimu.7Usidashangaa ndande ndida kukambila, ndi lazima ubadwe mala ya kawili. 8Mphepo ivuma palichocnhe yapoikonda ndi sauti yake muivela, nampho simuchiwa uko ichoka wala uke ipita. Ndeuma ili hali hali ya kila uyowabadwa ndi mzimu.9Ni kaddema wadanchibu, kokamba, "vinthu ivi vikhozekana bwanchi?" 10Yesu wadanchibu, "iwe uli puzisi wa Israeli, ata siunchidwa vinthu ivi?" 11Uzene, uzene, ndi kukambila chicha tuchinchiwa tuchiikila umboni kwa chicha tachiana.Nampho siwalandila umboni wanthu.12Ngati namkambila vinthu va yapa pa nchika ndi simukhulupalila, simkhoze bwanchi kukhulupalila ngati ndikokambilani vinthu va kumwamba? 13Pakuti palibe uyowakwela pamwamba kuchoka kumwamba ila iye wanchika, mwana wa mwanadamu.14Ngati muncha Musa umowadanyakula nchaka papururu, mchimwecho mwana wa mwanadamu lazima wainulidwe, 15ili kuti onche anyiwo siakhulupalile apate umoyo wa muyaya.16Pakuti kwa namna ii Mulungu wadalikonda jhiko, kuti wadamchocha mwana wa chisamba, ili kuti munthu waliyonche wamkhulupalila siwadangamia ila wakhale ndi umoyo wa muyaya. 17Ndande Mulungu siwadamtume mwana wake panchika ili wahukumu nchika, ila kuti nchika lilamichidwe mkati mwa iye. 18Uyowamkhulupalile iye siwahukumidwa. Uyo siwamkhulupalila tayari wanthohukumidwa ndandesiwadakulupalile nchina la mwana wachisamba wa Mulungu.19Iii ndo ndande ya hukumu, ya kuti dangalila lancha panchiko, nampho wanadamu udakonda mdima zaidi ya dangalila ndande vichito vao vidali vachimo. 20Kila munthu wachita voipa waliipila dangalila ili vichito vake sividancha kuikidwa wazi. 21Nampho, iye wachita bwino wakuncha kudangalila ili vichito vake vionekane kuti wachitika kwa kumvechela Mulungu.22Baada ya yamena, Yesu pamonchi ndi opuzila adapita pakati pa nchika la Yudea, kumeneko wadatumi muda pamonchi nao wamata batiza. 23Chipano Yohana nayo watabatiza kumeneko ku Ainea kalibu ndi Salim pakuti kudali ndi manchi ya mbili pancha, wanthu amancha kwake ndi kubatiza, 24Pakuti Yohana wadakali asapenyedwe kujela.25Ndeyapo padachokela mabishano pakati pa opuzila Yohana ndi Wayahudi kuhusu sikukuu ya kuchukidwa. 26Adapita kwa Yohana kumkambila, "puzisi, iye udali nayo nchidya la mnchinche Yorodani, iye wadashuhudia mau yake, penya wabatiz ndi onche apita amnchata."27Yohana wadanchibu munthu siwakhoza kulandila chinthu chalichonche ingakhale ngati waninkhidwa kuchoka kumwamba. 28Anyiimwa mwachinawene mushuhudia kuti ndi dakamba kuti, "ine osati Kristo, badala yake ndidakamba, ndatumidwa pachogolo pake."29Iye wali ndi bibi arusi ndi mbuye arusi chipano bwenchi wa mbuye arusi, waima ndi kuvechela chimwemwe sana ndande ya sauti ya mbuye arusi chipano ndi chimwemwe changa chakamilika. 30Wafunikana kuzidi, nane nifunikana kupungua.31Iye wachoka pamwamba, wali pamwamba pa yonche. Iye wali wa panchiko wachaka panchiko ndi wakamba vinthu va panchiko. Iye wachoka kumwamba wili pamwamba pa yenche. 32Iye washuhudia yancha wayaona ndi kuyavela, nampho palibe walandila ushuhuda wake. 33Iye walandila ushuhuda wako wahakisha kuti Mulungu ndi mzene.34Ndande iye watumidwa ndi Mulungu wakamba mau ya Mulungu pakuti siwaninkha mzimu kwa chipimo. 35Tate wamkonda Mwana ndi walinao umoyo wa muyaya, nampho kwaiye siwamvela mwana pamwamba pake. 36Iye wamkulupalila Mwana walinao umoyo wa muyaya, nampho kwaiye iwamvela mwana siwauona umoyo, ila asila ya Mulungu igwilizana pa mwamba pake.

Chapter 4

1Yesu yapo wadajiwa kuti Afasiri afarisi ajiwa kuti Yesu wali ndi omphuzila ndi kubatiza kuposa Yohana, 2(ingakale Yesu mwenye siwama batiza ila omphuzi na wake), 3wadachoka ku Yudea ndi kupita Kugalilaya.4Kwaicho kudali mate kupitila Kusamaria. 5Ndi wadafika mujhi wa Samaria, uo utanidwa Sikari, paupi ndi liwala ilo Yakobo wadampacha mwana wake Yusufu.6Ndi chitime cha Yakobo chidali pamenepo, Yesu wadali walema chiukwa cha ulendo ndi wadagona pafupi ndi chitima. Idali nyengo ya usana. 7Wamkazi wa Kusamaria wadaja kutunga majhi ndi Yesu wadamkambila, "ndipache majhi ndimwe." 8Ndadnda omphuzira wake adapita kumzinda kukagula chakudya.9Yuja wamkazi wadamkambila, "ikala bwanji iwe Muyahudi, kundipempha ine wamkazi Msamaria, chinthu cha kumwa?" Ndande Ayahudi siavanichana ndi Asamaria. 10Yesu wadayankha ngati ukadajiwa mphatso ya Mulungu, ndi yuja wakukambila ndi pache majhi, nkadamuphempha, ndiwadakuninkha majhi yopeleka umoyo.11Wamkazi wadayankha, "bambo mulije msomelo utungila majhi ndi chiteme ndi chonyowa, siuyapata kuti majhi ya umoyo. 12Bwanji iwe ndi wamkhulu, kuposa atate wathu a Yakobo, iye wadatininkha chitime ichi?"13Yesu wadayankha, waliyenche uyo siwamwe majhi yaya siwaonancho tujho, 14Nampho waliyenche uyosiwamwe majhi yayo sinimpache ine siwaonancho lujo. Pambuyo pake majhi yayo sindimpache siyakale ngati mchogololo umwaza majhi muyaya.15Yuja wamkazi wadamkambila, Ambuye, ndiyaona majhi yameneyo kuti ndisakale ndi lujo, ndi kuti ndisachanchika kuja pano kutunga majhi. 16Yesu wadamkambila, "pita kamtane mmunako, ndi ujhe."17Wamkazi wadamkambila, "ndilije wa mmuna. Yesu wadayankha wamkamba bwino ulije wammuna. 18Pakuti ulindi wa chimuna asano, ndi mmojhi ulinayo sazino osati mmunako. Yapa wakamba uzene."19Wamkazi wadamkambila, "abwana ndiona imwa ndi alosi. 20Achatoto watu amapemphera pa phili ili, nampho anyaimwe mkamba Kuyerusalemu ndo malo wanthu afunika kupemphela."21Yesu wadayankha, "wamkazi ndi kulupalile, nthawi ifika iye simupempha Ambuye pa pili lino kapena Kuyerusalemu. 22Anyaimwe wanthu mlambila icho simuchijiwa nampo ife tilambila icho tichijiwa, ndandeno mboli uchokela kwa Ayahudi."23Atachimwecho sije nyengo, ndi sazino ulipano nyengo anyiao alambila uzene salambile atate mumzimu ndi uzene ndande atate wauna una wanthu amtundu, umeneo kukala wanthu wake yao amlambila. 24Mlungu ndi mzimu, ndi anyiwaja amlambila afunika kumlambila kimzimu ndi zene.25Wamkazi wadamkambila, "ndijiwa kuti wakuja Mpulumusi, (watanidwa Kristo). Iye yapo siwaje siwatikambile yonche." 26Yesu wadamkambila, "ine ukamba nane nde iye."27Nyengo imweyo omphuzila wake adabwela nao adazizwa ndande chiyani wakambana ndi wamkazi, nampho palije uyo wadaesa kumafuncha, ufuna chiyani? Kapina, "ndande chiyani ukamba ndi uyu?"28Kwaicho wamkazi wadausiya mchukho wake ndi kupita kumzinda ndi kwakambila wanthu, 29"majani mpenyo munthu wandikambila nkhani zanga zonche izo ndazichita, bwanji ikozekana kuti nde Kristo?" 30Adachoka kumzinda ndi kuja kwaiye.31Nyengo ya usana omphuzila wake adamupempha ndi kukamba, Apuzisi idyani chakudya. 32Nampho iye wadaakambila, ine ndili ndi chakudya icho simuchijiwa anyaimwe. 33Omphuzila adakambilana, palije uyo wampacha chinthu chalichonche kudya, "bwanji adapeleka?"34Yesu wadakambila, chakudya changa ndi kuchita mafuno ya iye uyo wanditumiza ndi kwakanicha nchito yake. 35Bwanji simkamba kuti ikali miezi isano ndi zokololedwa zisikale zakwana? Ndikukambilani penyani minda umoili yakwanila kukolola. 36Uyo wakotola walandila mkokolo ndikusonkhanicha vipacho ndande ya umoyo wa muyaya, kuti uyo wavyala nayenche wakotola kuti akondwelele pamoji.37Pakuti mkambo uwu ndi zene, mmojhi wavyala ndi mnjake wakolola. 38Ndidakutumani kukolola icho simdagwile nchito, wina achita nchito ndi anyaimwe mkati mwa chisangalalo cha nchito yao.39Asamaria ambili pa mzinda uja adamkulupalila chiukwa cha wamkazi yuja wamatilila umboni nkhani zake, wadanikambila vonche ivo ndidavichita. 40Kwaicho Asamaria yapo adaja adamphempha kuti wakhale, nao ndi wadakala kwa anyaio masiku mawili.41Ndi ambili kupunda adamkulupalila chifukwacha mau lake. 42Adamkambila yuja wamkazi, "tukulupalila osati kwa mau yakope, ndande tachinawene tavela, ndi chipano tijiwa kuti iyende mpulumusi wa jhiko."43Pambuyo pa masiku ya wili wadachoka kupita Kugalilaya. 44Ndande iye mwene wake wadatolengeza kuti mlosi walije ulema kumuji wake mwene. 45Yapowadaja kuchokela Kugalilaya, a Kugalilaya adamlandila, adaona vinthu vonche ivo wadavichita Kuyerusalemu kuchisangalalo.46Wadajancho ku Kana ya Galilaya, kumeneko wadang'anamuka majhi kukala vinyo. PAdali ndi wamkulu iye mwana wake wadali odwala Kukapernaumu. 47Yapowadavela kuti Yesu wadachokela ku Yudea ndi kupita Kugalilaya, wadapita kwa Yesu ndikumupempha wachike wamuchirise mwana wake, uyo wadali paupi kumwalila.48Nde Yesu wadamkambila, anyaimwe mkasia osaone chizindikiro ndi vodabwicha simu ngate kukulupalila. 49Nduma wadanena, Ambuye chikani panchi mwana wanga wakaliosamwalila. 50Yesu wadamkambila mapita mwana wako wa moyo, yuja munthu wadakulupalila mau wadakamba Yesu ndi wadapita.51Yapo wamachikha, anchito wake adamulandila ndikumukambila mwana wako wadali wa moyo. 52Kwaicho wadaauncha mwachira nyengo yanji? Adayankha, julo nyengo ya saa saba nthenda idamusia.53Nde atate wake adajiwa kuti ndi nyenbo imweija wadakamba Yesu. Mwana wako walama kwaicho iye ndi amnyumba mwake adakulupalila. 54Ichi chidali chizindikilo cha kawili wadachita Yesu yapo wadachoka Kuyudea kupita Kugalilaya.

Chapter 5

1Pambuyo yapamene padasi ndi sikuku ya Wayahudi, ndi Yesu wadakwela kupita Kuyerusalemu. 2Ndikuja Kuyerusalemu padali ndi bikila pakoma pa mbelele, ilo limatanidwa kwa lukha ya Kiibraniya Bethzatha, nalo lili ndi vikhao visano. 3Wandhu ambili odwala idalipo, sapenya, anyao adalumala adali agona makundi yayo chatilila. (Mau ya mzele waka 3 siyaonekana katika nakala ya bwino na kale amalindila maji kuvundulidwa). Kolongosola ndawi yakuti angelo wadachika mnyumba mwa Mbuye ndi kuyavundula maji. 4Ndiposo yuja wadili oyamba kulowa mnyumba mwa badue maji kuvundulidwa wachitidwa kuvundulidwa wachitidwa kulama kuchokana ndi chilichonje chidali chamgwila ndawi imeneyo.5Ndi mundu mmoji wadali wadwala kwa vyaka 38 wadali mkati mwavi ngao. 6Yesu yapo wadamuona wagona mnyumba ya vigawo ndi baada yojiwa kuti wagona paja pandawi yaitali Yesu wadamkambila, "Bwa ukonda kulama?"7Yuja odwala wadayanga, "Ambuye nilibe mundu, wakuniika mbilika yaoi maji ya vunduka, yapo niesa kulowa mundu mwina wanichogolela." 8Yesu wadamkambila, "ukandi utenge tandiko lako upite."9Popo yuja mundu wadalama, wadatenga chitanda chake wadapita ndi siku limenelo lidali siku la sabato.10Chocho Ayahudi wadakambila yuja mundu walamichidwa, "lelo ndi siku ya sabata, ndi siuvomelezedwa kutenga tandiko lako." 11Wadayanga, iye wanilamicha nde wanikambila, "tenga tandiko lako ndiupite."12Adaunja, "ndiyani wakukambila utenge tandiko lako upite?" 13Ngakale, yuja wadalamichidwa, siwada mjiwe, pandande Yesu wadali wachoka kwa chisisi pakuti kudali ndi wandu ambili pamalo pamenepo.14Pambuyopo Yesu adampeza yuja mundu mnyumba ya Mbuye wadamkambila, "penya, walama! Usidachita machiminjo usidaja kupatidwa ndi machimo loipa kupunda." 15Yuja mundu wadapita kwanikha ngani Wayahudi kuti Yesu ndeuyo wamlamicha.16Chocho pandande ya vindi vimene Wayahudi adammenya Yesu, pandande wadachita vindu ivi siku la sabato. 17Yesu wadakambila, "Atate wanga apata njito mbaka chopano nane ndi chita njito." 18Pandande imeneyo Ayahudi adapunda kuunauna ili ampe opande pe pandande ya kuityola sabato, ndipo kwakutana Mulungu atate wake, wamajitita kuti walingana ndi Mulungu.19Yesu wadayankha, "mvomele, mvomele, mwana siwakoza kuchita chindu chalichonje ingakale chinja ambacho wamwona atate wake wachichita, pakuti chilichonje tate wachichitacho ndipo ndimwana siwachichite. 20Pakuti atate akonda mwana, ndi amulangiza kila chindu ichoachichita ndi samulangize vindu vavikulu kuposa yaya ndipa kuti muzidi kudabwa."21Pakuti ngati vija ambavo atate wanchavo wandu akua ndikwanikha umoyo, chocho mwananjo kunikha walionje wamkondwe. 22Pakuti atate siatoza walionje, ndipo wanikha mwana kutoza konje. 23Ndipo kuti onje amulemekeze mwana ngati vija mwana ivo walemekeza atate. Iye uyosiwalemekeza mwana siwalemekeza atate yao atuma.24Vomelani, vomelani, iye wavelae mau langa ndikuvomeleza iye uyowanituma walinao umoyo wa mtendele ndisiwatozedwa. Pambuyo pake, wapita kuchoka kunyifa ndi kulowa muufumu.25Vomelezani, vomelezani, nikukambilani ndawi ibwela ndi chopano ulipo uwo akua siavele mau ya mwana wa Mulungu ndioje yao savele salame.26Pakuti kuti vija atate ivo ali ndi umoyo mkati mwake mwene, 27chocho wanikha mwana kukala ndi umoyo mkati mwake, nditate wanikha mwana madalaka ili kuti walamule pakuti ndi mwana wa Adamu.28Msidadibwichidwa ndi ichi, pakuti ndawi ibwela ambao wakua onje yao alimviliza savele sauti yake, 29nao sachoke kubwalo kwa yao achita vabwino kwa kuchidwa kwa mtendele ndi yao achita voipa kwa kuuchidwa kwa kulamulidwa.30Sindikoza kuchita chindu chilichonje kuchoka kwanga namwene. Ngati umo ndivelela, chocho ndenilamula ndi kulamula kwanga ndi ya uzene pakuti sndiuna chikondi changa, bali chikondi chake uyo wanituma. 31Ngati sindijakambile namwene, upungu wanga siudakakala wauzene. 32Kuli mwina uyo wayaona kuhusuine ndijiwa pauzene uzene uwo wauwona ndi wauzene.33Mwamtuma kwa Yohana nae waivomeleza uzene. 34Hata chocho, uzene uwo ndiulandila siuchokha kwa mundu ndiyakamba yaya kuti mkoze kupulumuchidwa. 35Yohana wadali ndinyali iyoidali kwakundi kungala, ndimudali ovomela kuisekelela pandawi yaitali mulu yake.36Uzene ndilinao niwaukulu kuposa uja wa Yohana, panjito izo atate andipacha kuzimalizila, njitozo ndizichatazo zivomeleza kuti atate andituma. 37Atate yao andituma iwo wene apenya kuti ine simudawai kuvela mau yao wala kuliona umbo lake ndawi iliyonje. 38Palibe mau lake likakala mkati mwanu pakuti simumkulupilila iye watumidwa.39Uyo mumchunguza malembo ndi muganiza mkati mwake muli ndi umoyo wa mtendele, ndi yayo malembo yavomeleza khani yanga ndi 40wimufuna kubwela kwanga ili mpate umoyo wamtendele.41Msidalandila sifa kuchoka kwa wandhu, 42nambo ndijiwa kuti mulibe chikondi cha Mulungu mkati mwanu anyiimwe mawene.43Adabwela pajina la tate wanga, simudakoze kunilandila ngati mwina yapo siwaike pajina lake muda kumlandila. 44Bwa, mkoza kuvananavo anyiimwe ivo mulandila sifa kuchoka kwa kila mmoji wanu nambo simulandila sifa kuchoka kwa Mulungu wa yoka?45Musadakhaniza ine sindikumangene pachogolo patate. Yao akumangani anyiimwe ndi Musa, uyo anyiimwe mwamuika chifuno chanu kwake. 46Ngati mmakakala muvananavo va Musa, simudakananavo vaine pandande wadalemba kulingana ndi khani zanga. 47Ngati simuamini malembo yake, simukoze bwanji kuvananavo malembo yanga?

Chapter 6

1Pambuyo pankanizi Yesu wadaenda pampepete za Galilaya, ota chimwecho itanidwa nyanja ya Tiberia. 2Msonkano waukuru adali mkumchata chifuko adaona chilangizo wamachichita kwa achaamene adali odwala. 3Yesu wadakwela pamwamba kusikwa pamwamba papili ndi wadakala kumeneko ndi oyaruzidwa wake.4(Ndi Pasaka,sikuku ya Ayahudi idali ndi iwandikila). 5Yesu yapowadakweza maso yake kwamba ndikuona lintu lambili uli mkuja kwaiye wadamkambila ilipo sitipite kuti kukagwa mikate dala anyiyawa akoze kudya? 6(Nampo Yesu wadayakamba yaya kwa ilipo pakumuyesa chifukwa iye mwene wake wadajiwa icho siwachidie).7ilipo wadayankha, "ata mikate ya ndekana anike siungakoze kulamicha wanthu wonche ingakale waliyenche wakada peza pang'ono." 8Andrea mmoji wa oyaluzidwa wake m'bale wake Simoni Petro wadamkambila 9Yesu "kuli mnyamata pano wali ndi mikate isano ndi nchomba ziwili nampho siitandize chiyani kwa wanthu ambili ngati anyiyawa?"10Yesu wadamkambila, "akazikeni panchi wantu" 11Pambuyo Yesu wadatenga iji mkate isano ndi kuyamika ndi kwa agawila anyiwaja adakala panchi chimoji maji wadanagawila nchomba kwa mmene adafunila. 12Wanthu yapo adakuta wadaakambile ajiyaluza wake viikeni limoji vodulidwadulidwa vokala vokalila dala kuti sichidataika chilichonche.13Mmwemo adaviikila limoji ni kutila misece iwili vodulidwa va mikate ya nganovidachurukila ndi achameneo adadya. 14Pambuyo wantu yapo adapenya ine chitidwe ya chilangizo adanena "chazene uyunde yuja olosu." 15Yesu yapo wapo wadajiwa kuti ameuna kumgwira dala kuti amchile umu wao wadajiike pamphepete ndiwadapita kupiri iye yeka.16Yapo idali ujulo oyaluzidwa wake adachika kupita kunyanja. 17Adakwera mbwato ndi amayo mboka kupita Kukapernaumu. (Mdima udalowa ndi Yesu wadali wakali osaika kwa anyaiwo). 18Ntawi imeneyo mpepo ya mpavu idali mkupepeta ndi nyanja idali ndi inyendekela kuwangika.19Ndipancho oyaruzidwa wake pamene amapalasa nkafi ngati ishirini ndi zisano kapena thelasini adamuone Yesu ndiwayenda pamwamba panyanja kuwandikila bwato ndi adaopa. 20Nampo wadaakambila, "ndiliine msada ndiopa." 21Ndiponcho adakala ajikonja kumbara mbwato ntawi yomweyo apeze bwato waika kujiko limenelo anapita.22Siku limechatira msonkhano udaima kumpepete mwanyanja ndi adepenya kulibe bwato ulionche ikapanda umweija Yesu ndi oyaluzidwa wake siada kwelemo nampo oyaruzidwa wake adapata achinawene wake. 23(Ingakale padalipo mbwato yochepa kuchokela Tiberia paupi ndi malo amadyela mikale pambuyo umu kuchocha mayamiko.)24Ntawi msonkhano yapo udajiwa kuti osai Yesu ingakale oyaruzidwa wake adali kumeneko nchuke wene wake adakwera mkati mamabwato adapita kukapera nami kupita ndia muneune Yesu. 25Pambuyo pakumpeza maloyena yanyaiya adamfuncha, "Rabi udajaliti kuno?"26Yesu wadayankha wadaakambila chazene mundifunefune ine. Osati chiukwa mdeona malangilo nampo ndande mdedya mikate ndi kukuta. 27Siani kuchilichitila nchito chakudya eno wanangika nampo mchitile chito chakudya cholana ntawi zonche chija chimene mwana wa muntu siwakupacheni chifuko cha Mulungu tate waika chizindikililo pamwamba pake.28Pambuyo anamkambila, "chiyani tiunka kuchita dala kwachita nchito za Mulungu?" 29Yesu wadayankha, "indechito ya Mulungu kuti mumukurupalile iye watanidwa."30Mmwemo adamkambila, "ndi chizindikililo chiti chimene ukoza kuchita dala tichione ndi kukurupalila? Siuchite chipalilo? 31Achaatata watu adadya mkate pandanga ndenga ngati mmene idalembedwela wadaapacha mikate kuchokela kumwamba dala adye."32Pambuyo Yesu wadayanka, "cheza chazewa osati Musa wadaapacha mikate kuchokela kumwamba ikapanda atate wanga nde mmeneyo wakapechani mikate yazwe kuchokela kumwamba. 33Pakuti mkate wa Mulungu nde uja uchika kuchokera kumwamba ndi kumpacha mtendele jiko. 34Adamkambila, "umu tipache mkate umeneo ndawi yonche."35Yesu wadaakambila, "ine nde mkate wa mtendele imene siwaje kwaine siwapeze njara ndi mnene siwakulupalileswapeze rujo." 36Ingakale ndidakukambilani kuti mwandione ndi mkali osadiona. 37Wonche achameneo atate andipacha siaje kwanga ndi waliyenche siwaje kwaine sindi msia kubwalo.38Chifuko ndechika kuchokela kumwamba osati yuja kuachita voune vanga ikapanda vochita vaiye wandipacha utenga. 39Ndiyaya ndiyo yoana yake mwene wandipacha utenga kuti ndi sadamtaya mmoji waacha ameneo wandipacha ikapaga sinde abweze kumanda ntawi yotela. 40Chifuko ichi ndicho chofuna tata wanga kuti waliyenche wampenya mwana ndi kumkulupalila wakale ndi mtendele woseta nanencho sindimbweze kuwanda ntawi yotela.41Pambuyo pake Wayahudi adamdandaulila kupande iye chifuko wadakamba ine nde mkate wachika kuchokela kumwamba. 42Adakamba, "uyu si Yesu mwana wa Yusufu, mme tata wake ndi mayi wake timjiwa? Ikara bwanji chapano wakamba, nde chika kuchokera kumwamba?"43Yesu wadayankha wadaakambila msada dandaulane mmalo mwanu mwa achinawene wake. 44Palije munthu siwaje kwaine popande kukokedwa ndi tata wanga wandhu pacho utenga nanencho sindimbweze kumalo ntawi yotela. 45Chifuko yalembedwa mwaolopi, "siyaluzidwe ndi Mulungu." aliyenche wavela ndi wajiyaluza kuchokela kwa tata watu wa kuja kwaine.46Osati kuli Mulungu wamuone tate ikapanda mmene wachokela kwa Mulungu wamwe one atate. 47Zindikileni wadakilani waliyenche wa kulupalila wali ndi mtendele wosata.48Inende mkate wa mtendele wosata. 49Acha atate wanuadadya mikate pandenga danga ni adamwalila.50Uu ndi mkati uchika kuchokela kumwamba dala kuti wadyeke malo yake dala siwadamwalila. 51Ine ndi mkate ulama umeneo wachika kuchokela kumwamba ngati munthu waliyenche siwadye malo yamkate uu siwalame vyaka vonche mkate sindiuchocho ndi tupi langa chiuko cha kakanidwe kajiko.52Ayahudi adakwiyilama achinawne ndi adayamba kukangana ndi akamba muntu uyu akoza bwanjo kutipacha tupi lake tidye? 53Pambuyo Yesu wadaakambila, zindikilani ngati simudya tupi la mwana wamuntu ndi kuwa mwazi wake simkala ndi umoyo wosata mkati mwanu.54Waliyenche wakudya tupi langa ndi kumwa mwazi wanga wali ndi umoyo wosata nanencho sindi mchocho kwanda ntawi yotela. 55Pakuti tupi langa ndi chakudya chazene mwazi wanga ndi chomwela chabarimu. 56Mmene wakudya tupi langa ndi kuwa mwazi wanga wakala mkati mwanga nanencho mkati mwake.57Ngati atate ali ndi mtendele mmenemo anitumizila ine nde ngati umo ndili chifuko cha atate nayenche siwalame chifuko chaine. 58Uu nde nde mkate uchika kuchokela ku mwamba osati ngati mmene adadyela anya atate ndi kumwalila mmene wakudya mkate uu siwakale ndi malamedwe yosafa. 59Yesu wadakamba mau yaya mkati mwa koyumba ya Mulungu pamene wame yaluza kumene Kukapernaumu.60Nde pamenepo oyaruzidwa wake ambili adavela yaya adakamba, "ili ndenyaluzo lolimba yani wakoze kumlandila?" 61Yesu chiuko wadajiwa kuti oyaluzidwa wake adandaulila nkani iyi adawauncha bwanji nkani iyi ya kudandaulichani?62Chapano siikale bwanji mkamwona mwana wa muntu ndiwachika kuchokela ukoesdsli mmayambo? 63Mzimu ndi umeneo uchocha mtendele tupi silitandazika chilichonche mau neya kamba kwanu mtima ndi mtendele.64Mkali pakati panu amene sialolela." Chifukwa Yesu wadajiwa chiyambile mmayambo mwene yuja siakoze kulolela ndiye mmeneyo siwasanduke. 65Wadaakambila ndi chifukwa chake ndidakukambilani kuti palibe muntu wakoze kuja kwaineingakale wapelekedwa ndi atate."66Pambuyo payameneyo oyaruzidwa wake adabwela mmbuyo ndi siada chatane nayencho kukalila limoji naye. 67Yesu wadaakambila anyiwaja makumi ndi awili, "bwanji anyiimwe mufuna kuchoka?" 68Simoni Petro wadayankha, "bambo tipite kwa yani mbona imwe mulinayo mau ya malamidwe yosata, 69ndi favananavo ndikujiwa kuti iwe ndi muntu oyela wa Mulungu."70Yesu wadaakambila bwanji ine sindidakusankuleni anyiimwe ndi mmoji wanu si wabwino? 71Chapano wa makambila nkani ya Yuda mwana wa Simoni Iskariote, chifukwa wadali iye wali mmoji wa anyiwaja kumi ndi awili mmene wa mafune mzukira Yesu.

Chapter 7

1Pambuyo pa vichito ivi Yesu wadasairi chimwechi pa Galilaya kwa chifuko siwadaune kupita Kuyahudi kwa chifuko Wayahudi kwa chifuko Wayahudi adali kuchita pagho pangho za kumpha. 2Chipano sikukuu ya Wayahudi, sikukuu ya vibanda idali pafupi.3Ndipo achabalewake yapo adamkambila, "choka pa malo pano upite Kuyahudi, kutiopinzila wako chimwecho avione vochita ivo uvichita. 4Palijhe wachita chalichonche kwa chisiri nati iye mwene wake wauna kuzindikilidwa poyera ngati uchita yameneyo jilangize wa mwene kwa jhiko."5Ingakale achabale wake nao siadamkulupalile. 6Ndipo Yesu adawakambila, "nyengo yanga sida walandikile ikali nampho nyengo yanu kila kaka nyinji uliokonjeka. 7Jhiko silikoza kukuipilani anyiimwe ikapanda uniipila ine chiuko sinichile umboni kuti vochita vake ndi voipa.8Kwelani kupita kusikukuu, ine sinipita pa sikukuu iyi kwa chifuko nthawi yanga siudakwanile ukali." 9Pambuyo pakunena yameneyo kwa anyaiwo, wadakala Kugalillaya.10Ingakale chimwecho achabale wake yapoadali kupita kusikukuu, ndipo iye naye wadapita osati kwa danga nampho kwa chisiri. 11Wayahudi adali kumfunaf pa sikukuu, uku na nena, "walikuti?"12Kudali ndi kupachana maganizo ya mbili mmalo mwa opezana pamwamba pa iye. Wena adanena, "iyayi wasokhaniza ovechela." 13Ingakale chimwecho palibe uyo wadakamba mo masuka pa iye kwa kuwa wopa Wayahudi.14Nyengo sikukuuyapoidaika pakatikati, Yesu wadakwela kupita kuhekaluni ndi kuyamba kuyaluza. 15Wayahudi adali ozizwa ndi kunena, "kwa mtundu uti munthu uyu wajhiwa vichito vya mbili? Siwadapunzile nditu?" 16Yesu wadayankha ndi kwakambila, "mayaluzo yanga osati yanga ikawa ndi yake iye wantume."17Ikakala waliyenche siwakonde kuchita chikondi chake iye, siwajhiwe yayo mayaluzo yameneyo ngati yachoka kwa Mulungu, kapena ngati ninena kuchoka kwa ine namwene. 18Waliyenche wanena yachoka kwa iye mwene waunauna ulemelelo wake. Ikapanda waliyenche waunauna ulemelelo wake iye wamtuma mundhu mmeney ndi wa zene, ndi mkati mwake mulijhe popande kuchita malinga.19Musa siwadakupacheni anyiimwe matauko? Nampho palijhe ata mmojhi pakati panu wachita malinga. Kwa ndande chiyani muna kumpha? 20Okomana adayankha, "uli ndi vilombo. Yani waune kukupha?"21Yesu wadayankha ndi kumkambila, "nachita nchito imoji anyiimwe mwawonche mwazizichidwa kwa chiuko chake. 22Musa wadakupachani jhando (osati kuti ichoka kwa Musa, ikapanda ijha ichoka kwa matate), ndi pa sabato muyenelela mundhu.23Ikakala mundhu siwalandile jhando musiku ya sabato kuti matauko ya Musa isadawanangika. Kwa chiuko chanji munikwiha ine. Ndande namchita mundhu kukala wa moyo nditu pa Sabato? 24Msadalamula kulingana ndi maonekeledwe, ikawe lamulani kwa Malinga.25Ikumjhi yewo achoka Kuyerusalemu adanena, "osati uyu amunauna kumpha? 26Kapenyani wakamba pauyata yata ndi siakamba chalichonche pamwamba paiye sikozekana kuti ochogoza ojhiwa zene kuti uyu ni Kristo, ikozekana kukala? 27Tijhiwa uyu mundhuwachokela kuti. Kristo yaposiwajhe atachimwecho, popande siwamjhiwe kuti wachokela."28Yesu wadali mkukuza mau yake muhekaluni, ndiwayaluza kunena, "anyiimwe mwawonche munijhiwa ine ndi munijhiwa ukondichokela. Sinidajhe kwa mzimu wanga, ikawe kwa iye wanituma ndi wazene, ndi simunijhiwa iye. 29Nimjhiwa iye kwa chiuko nachokela kwa iye ndi wadanituma."30Adali kumuyesa kumgwila, nampho palibe yata mmojhi wadakweza janjha lake kumwamba kwake chifuko ntawi yake idali ikaki kuwalandikila. 31Ata chimwecho, ambili pa msughano adamkulupilila. Kunena, "Kristo yaposiwabwele siwachite vizindikilo vambili kusi yana izo wazichita mundhu mmeneyo?" 32Mafarisayo adavela agulundianong'onezana ghani iyo imkuza Yesu, ndi wakulu wakulu anchembe ndi mafarisayo adatuma olemelela kuti amgwila.33Ndipo Yesu wadanena, "kukali nyengo yosapitilile nili pamojhi panu, ndi pambuyo sindipite kwaiye wanituma. 34Simnifunefune nampho simuniona; kumene nipita, simkoza kupita."35Kwa icho Wayahudi adakamba na anyiiwo kwa anyiiwo, "mundhu uyu siwapite kuti kutisitidakoza kumwona? Siwapite kwa asoganichidwa pakati pa Wayunani ndi kuwayaluza Wayunani? 36Ndi mau diti ili wanena, simnifunefune, nampho simniona; kujha nipita simkhoze kujha?"37Chipano pa masiko yotela, siku yaikulu ya sikukuu, Yesu wadaima kukuza mau, kunena, "ikakala waliyenche wasi ndi lujho, wajhekwaine wamwe. 38Iye wanikulupalila ine, ngati malembo umowanenela, kuchoka mkati mwake sigugume michinje ya majhi ya umoyo."39Nampho wadayanena yaya kukuza mzimu, uyo anyiiwo amkulupalila siwamlandile; mzimu udaliukali kuchechedwa kwa ndande Yesu wadali avali siadakuzikidwe.40Akumojhi agulu, yapoadavela mau yaya adanena, "zene uyu ni olosa." 41Wena adanena, "uyu ndi Kristo." Nampho wakoze kuchokela Kugalilaya? 42Malembo siyadanene kuti Kristo siwachokele pa kamu la Daudi, ndi kuchoka Kubeyhelehemu chijhijhi icho Daudi wadali?43Mmwemo, pajha padachokela chitengano pakati pa magulu kwa chifuko cha iye. 44Wena pakati pawo adakagwila, nampho palibe uyowadaongola manja yake pamwamba pake.45Ndipo anyiwajha olemelela adabwela kwa wakuluwakulu anchembe ndi Maarisayo nawo adankambila, "kwa ndande yanji simdabwele naye?" 46Olemelela adayankha, "palijhe mundhu wadapeza kukamba ngati uyu mmayambo."47Ndipo Mafarisayo yapoadayankha, "ndi anyiimwe namwe mwawanongidwa? 48Kuli waliyenche pa uyowamkulupilila, kapena waliyenche wa Mafarisayo? 49Ikapanda anyiyawa agulu siajhiwa matauko alwesedwa."50Nikodemo adamkambila (iye adamsendelela Yesu kale kakala mmojhi wa Mafarisayo), 51Bwanji matauko yatu yamlamula mundhu ikapande wavecheledwa poyamba ndi kujhiwa ichowachichita? 52Adayankha ndi kumkambila, "ndiine nawe uchokela Kugalilaya? Funafuna ndi uwone kuti palibe olosa wachokela Kugalilaya."53(Penyelela: Mwa mau ya Yohana 7:53 - 8:11 pa malembo yokadwa ya kale). Ndipo kila mundhu wadapita kukomo kwake.

Chapter 8

1Nampho Yesu wadapita kupili la mizeituni. 2Siku lidachatila umawa mawa wadapita kukanisa wanthu onche adamchata, wadakala ndi kuayaluza. 3Olemba ndi Maarisayo adampelekela wamkazi wadagwilidwa ndiwachita chigololo adamuika pakati.4Adamkambila Yesu apuzisi wamkaziyu wagwilidwa ndi wachita chigololo. 5Mu tauko la Musa wadatilamula kuabula myala wanthu amtundu wa iwe ukamba bwanji kwa munthuyu? 6Amakamba yaya kuti apeze chinthu chomwimbila mlandu, nampho Yesu wadakotama panchi ndi kulemba panchi ndi chala chake.7(Zingatia: Angalia ufafanuzi wa Yohana 7: 53 - 8: 11 hapo juu). Yapo adaendekela kumfuncha, wadaima ndi kuakambila uyo walije machimo mkati mwanu wakale oyamba kumponya myala. 8Wadakotamamncho panchi, ndi kulembancho panchi ndi chala chake.9(Zingatia: Angalia ufafanuzi wa Yohana 7: 53 - 8: 11 hapo juu).Yapo adavela chimwecho, adachokapo mmoji mmoji kuyambila okota, potela Yesu wadakala yoka pamoji ndi yuja wamkazi wadali pakatikati pao. 10Yesu wadaima ndi kumkambila, wamkazi, akuimba mlandu alikuti? Palije uyu wakulanga? 11Wadakamba palije ata mmoji, ingakale ine sinikulanga, mapita usakachitancho machimo.12Yesu wadachezancho ndi wanthu kukamba, "ine ndi dangalila la jiko la panchi, uyo siwanichate siwaenda kumdima nampho siwakale ndi dangalila la umoyo." 13Mafarisayo adamkambila, "ujichitila umboni wa mwene, umboni wako osati wa zene."14Yesu wadayankha, wadaakambila, ingakale nikajichitila umboni namwene, umboni wanga ndi zene nijiwa kumalo uko ichoka ndi uko nipita nampho anyiimwe simjiwa uko nichoka kapena uko nipita. 15Anyiimwe mulanga mwa thupiine sinimlanga waliyonche. 16Ine nikalanga, chilango changa chazene ndande sinili neka nampho mli pamojhi ndi atate yao anituma.17Ndi mmatauko yanu yalembedwa kuti umboni wa wanthu awili ndi wazene. 18Ine nde nijichila umboni, atate yao anituma anichitila umboni.19Adamkambila, atate wako ali kuti? Yesu wadayankha ine simnijiwa, ingakale atate wanga simuajiwa mdakali munijiwa ine, mdakaji wa ndi atate wanga. 20Wadakamba mau yaya cha kuikila yapo wamayaluza muhekalu ni palije ata mmojhi wadamgwila ndande nthawi idali siidafike.21Wadaakambiancho, nitopita simnifunefune ndi simfe mmachimo yanu, kuja nipita simkoza kuja. 22Ayuda adakamba, siwajipe mwene, iye wadakamba, "kuja nipita simkoza kuja?"23Yesu wadaakambila, "mchokela panchi, ine nichokela kumwamba, anyiimwe ndi ajiko lino la panchi ine osati wa jikolino la panchi. 24Kwa icho nidakukambilani kuti sime mmachimo yanu ngati simkulupilila kuli nde ine sime mmachimo yanu."25Adamuncha iwe yani? Yesu wadaakambila, yaja nidakukambilani chiyambile kale. 26Nili ndi vinthu vambili vocheza ndi kulanga kwa anyiimwe, ingakale chimwecho, iye wanituma ni wazene ni vinthu ivho navivela kuchoka kwa iye ine nivikamba kwa jiko la panchi. 27Saadavane nae kuti wakamba nao kukuza atate.28Yesu wadakamba, yapo simu mkuzika mwana wa munthu nde yapo simjiwa kuti ine nde iye ndi kuti sinichita chilichonche kwa mtima wanga, ngati umo atate aniyaluzila nde nicheza vinthu ivi. 29Iye wadanituma wali pamojhi ndi ine, ndi iye siwadanisiye neka, ndande kila nyengo nichita vija vinikondwelecha. 30Nyengo Yesu ndi wakamba vinthu ivi ambili adamkulupilila.31Yesu wadakamba kwa Ayuda adamkulupilila, ngati simkale mkati mwa mau langa simkale opunzila wanga azene, 32namwe simjuiwe uzene, uzene siukupacheni ufuru. 33Adamuyankha, ife vibadwa va Ibrahimu, sitakalepo panchi pa ukapoto wa walionche ukamba bwanji, simkale ndi ufuru?''34Yesu wadaayankha, "kulupililani nikukambilani kila uyo wachita machimo ndi kapolo wa machimo. 35Kapolo siwakala pakomo nthawi yonche, mwana nde wakala pakomo siku zonche. 36Kwa icho, ikakala mwana wakuchitani mafuru mkala mauru zenedi."37Nijiwa anyiimwe vibadwa va Ibrahimu: muna kunipa ndande mau langa lilije malo mkati mwanu. 38Nikamba vinthu ivo naviona pamoji ndi atate wanga ingakale anyiimwe mchita vinthu ivo mwavivela kuchokela kwa atate wanu.39Adayankha ndi kumkambila, "atate watu ndi Abrahamu." Yesu wadaakambila, mdakali wana wa Abrahamu mdakachita nchito za Abrahamu. 40Ine nakukambilani uzene nauvela kwa Mulungu, anyiimwe mfuna kunipa, Abrahamu siwadachite chimwecho. 41Mchita nchito za atate wanu, adamkambila, "sitidabalidwe mchigororo tili ndi tate mmoji Mulungu."42Yesu wadaakambila, ikakala Mulungu nde atate wanu mdakanikonda ine, ndande nachoka kwa Mulungu, sinidaje kofuna ine, iye nde wadanituma. 43Ndande chiyani simvananayo mau yanga? Ndande sinikoza kudikila kuvechela mau yanga. 44Anyiimwe ndi wa atate wanu, "Satana," ndi muna kuchita kumbilo la atate wanu. Wadali wakupa chiyambilepo ndi siwakoza kuima muuzene ndande uzene palijemo mkati mwake, yapo wakamba unami wakamba kuchokela mchiyambo chake ndande iye waunami ndi tate wa unami.45Chapano ndande nikambachazene sinikulupilila. 46Yani pakati panu wanichitila umboni kuti nili ndi machimo? Ikakala nikamba uzene ndande chiyani simnikulupilila? 47Uyo wali wa Mulungu wavela mau ya Mulungu anyiimwe simvechele ndande anyiimwe osati a Mulungu.48Ayuda adamuyankha, ndi kumkambila, sitidakambe zene kuti iwe ndi Msamaria ndi uli ndi vimphuza? 49Yesu wadayankha, nilipo vimphuza. Nampho nimlemekeza atate wanga, anyiimwe simnilemekeza.50Sinifunafuna kuyera kwanga, kuli mmoji wafunafuna ndi kulanga. 51Walionche uyo siwagwile mau langa siwakuona kufa.52Ayuda adamkambila chipano tajiwa kuti uli ndi vimphuza, Abrahamu ndiolosa adaa, nampho ukamba ikakala munthu siwagwile mau lako siwalawa kufa. 53Iwe osati wamkulu, ngati atate watu Abrahamu wadafa? Olosa adafa, iwe ujichita kuti yani?54Yesu wadayankha, ikakala nijikuzika namwene, kuyera kwanga ndi chaje, ndi atate wanga anikuzika, yuja mumkamba ndi Mulungu wanu. 55Anyiimwe simdajiwe iye, nampho iwe nimjiwa iye ikakala sinikamba, sinimjiwa sinikala ngati anyiimwe waunami, ingakale chimwecho nimjiwa ndi mau yake nayagwila. 56Atate wanu Abrahamu wadayangalilaumo siwaione siku yanga, wadaiona ndi wadali ndi chimwemwe.57Ayuda adamkambila siudaike vyaka makumi ya sano nawe wamuona Ibrahimu? 58Yesu wadaakambila, kulupililani nikukambilani Abrahamu wakati osabadwe INE NILIPO. 59Ndeyapo adatondola myala anibule, nampho Yesu wadajibisa ndi kuchoka kubwalo kwa hekalu.

Chapter 9

1Nyengo ngati Yesu yapo wamapita, wadamuona munthu osapenye kuyambila kubadwa kwake. 2Opuzila wake adamuncha, "apuzisi, yani wadachita machimo, munthu uyu, kapena obala wake mbaka wabadwe osapenye?"3Yesu wadaayankha, "osati uyu munthu kapena opala wake anyiyao adachita machimo, nampho ni nchito ya Mulungu zipate kumasulidwa kupitila kwake. 4Tifunika kuchita nchito zake iye wanituma nyengo ukali usana. Usiku ukajha nyengo iyo palibe uyo siwakhoze kuchita nchito. 5Nyengo nikhalapo pajhiko, ine ni dangalila la pajhiko."6Pamalo pa Yesu kukamba mau yaya, wadalavula padoti, wadachita thokope kwa malovu, ndi wadampaka yujha munthu mmaso ndi lijha thokope. 7Wadamkambila, mapita kasambe pachitime cha Siloamu (iyo ithandauzidwa ngati "uyo watumidwa"). Kwa chimwecho iye munthu wadapita, wadasamba, ndi walabwela niwapenya.8Apafupi ayujha munthu ndi anyiwajha adamuona poyamba ngati opempha adakamba, bwa uyu osati yujha munthu wamakhala ndi kupempha? Wina adakamba, "nde iye." 9Ndi wina adakamba, "notho, nampho walingana nae."Nampho wadakamba, "Nde ine."10Adakambila, "chipano maso yako yamasulidwa?" 11Wadayankha, munthu watanidwa Yesu wadachita thokope ndi kuyapaka maso yanga ndi kunikambila, mapita ku Siloamu ukasambe. Kwa icho nidapita, ndinidasamba, ndi nidapeza kupenyancho. 12Adamkambila, "wali kuti?" wadayankha, "sinijhiwe."13Adampeleka yujha munthu wadali osapenye kwa Afarisayo. 14Nayo idali siku la Sabato nyengo Yesu yapo wadakonja thokope ndi kuyamasula maso yake. 15Ndiponcho Afarisayo adamuncha wadakhoza bwanji kupenya. Wadaakambila, "wadaika thokope, mmaso mwanga nidasamba, ndi chipano nikhoza kupenya."16Wina wake wa Aarisayo adakamba, "munthu uyu siwadachoke kwa Mulungu kwa chifuko siwaighwila sabato." Wina adakamba, "ikhozekana bwanji munthu wa machimo kuchita langizo ngati ili?" Kwa chimwecho kudali ndi kugawana pakati pao. 17Nde yapo adamuncha yujha osapenye, "ukamba bwanji pakati pake kwa chifuko wadayamasula maso yako?" Osapenye wadakamba, "Ni oLosa." 18Ata nyengo ii Ayahudi adamvomela kuti wadali osapenye nae wapeza kupenya mbaka yapo wadaatana obala wake iye wadapeza kupenya.19Wadaauncha obala, bwanji uyu ni mwana wanu uyo mukamba wadabadwa osapenye? Wakoza bwanji chipano kupenya? 20Chimwecho obala wake adamuyankha "tijhiwa kuti uyu ni mwana wathu ndi kuti wadabadwa osapenye. 21Mtundu wanji chipano wapenya, sitijhiwa, ndi uyo wammasula maso yake sitimjhiwa. Muncheni iye ni munthu wamkulu wakhoza kujiotokoza mwene."22Obala wake adakamba vinthu vimenevo, kwa chifuko wadaopaAyahudi. Kwa mujha Ayahudi adali avomelezana tayali kuti ikakhala waliyonche siwavomele kuti Yesu ni Kristo, siwasankhidwe ni Sinagogi. 23Kwa ndande ii, obala wake adakamba, "ni munthu wamkulu, muncheni iye."24Kwa chimwecho kwa mala ya kawili, adamtana, yujha munthu wadali osapenyendi kumkambila, "mpache Mulungu tijiwa kuti munthu uyu ni wamachimo." 25Nde yujha munthu wadayankha, "wakhale wa machimo, ine sinijhiwa chinthu chimojhi icho nichojhiwa ; Nidali osapenye ndi saino nipenya."26Ndeyapo adamkambila, wakuchitila chiyani? Wadayamasula bwanji maso yako? 27Wadayankha, "nathokukambilani tayali, ndi anyaimwe simudavechele! Ndande yanji muna kuvelancho? Namwe simuna kukhala opuzila wake, osati? 28Adamtukana ndi kukamba, iwe ni opuzila wake, nampho ie opuzila a Musa. 29Tijhiwa kuti Mulungu wadakambana ndi Musa nampho kwa uyumunthu, sitijhiwa uko wachokela."30Yujha munthu wadayankha ndi kwa akambila, "kwa chiyani ichi ni chinthu chozizuucha, kuti sitijhiwa ukowachoka, ndi wayamasula maso yanga. 31Tijhiwa kuti Mulungu siwavechela amachimo, nampho ikakhala munthu waliyonche Mulungu ndi kuchita chikondi chake, Mulungu wamvechela.32Kuyambila kuyamba kwa jhiko siidachokele kuvechedwa kuti waliyonche wamasula maso ya munthu uyo wadabadwa osapenye. 33Ikakhala munthu uyu siwadachoke kwa Mulungu , siwadakachita chalichonche. 34Adayankha ndi kumkambila, "udabadwa pakati pa machimo kupunda,nawe utiyaluza ie?" Mdipo adamtopola kuchoka pakati pa sinagogi.35Yesu wadavela kuti amchocha msinagogi. Wadamchata ndi kumkambila, "umvomela mwana wa munthu?" 36Wadayankha ndi kukamba, "niyani, ambuye kuti nane nikoze kumvomela?" 37Yesu wadamkambila, "wathomuona, nayo uyoukana nayo nde iye." 38Yujha munthu wadakamba, "Ambuye navomela" ndeyapo wadamlambila.39Yesu wadakamba, "kwa lamulo najha pa jhiko lino kuti anyiwajha sapenya akoze kupenya ndi anyiwajha apenya akhale osapenya." 40Wina wake wa Aarisayo adali pamojhi nayo adavela mau yake ndi kumfuncha "ndi ife nafe osapenya?" 41Yesu wadaakambila, "ngati mdakakhala osapenya simdakakhala ndi machimo. Ata mchimwecho chipano mukamba, "tipenya," chimo lanu likhala.

Chapter 10

1Mvanenavo mvanenavo ndikukambileni, yujosiwalowa kopitila chicheko chokala la mbelele. Nampho wakwela kwanjila ina yake, munthu mmeneyo ndi mnkhungu. 2Iyo walowa mchicheko ndi oweta wa mbelele.3Kwake mlonda wa chicheko kumchukulila. Mbelele aivela sauti yake ndi kuzitana mbelele zake kwa majina yao ndi kwa choka kubwalo. 4Yaposiachoche kubwalo ali wake siachogoze, ndi mbelele siwaachate,aijiwa sauti yake.5Siamchata mlendo nampho pambuyo pake. Siamuyepuke, pakuti siazijiwa sauti za ulendo. 6Yesu wadakamba mfano huno kwao, nampho siadavielewe viatu niambavo wadali kuvikamba kwao.7Yesu wadakamba naoncho, "uvanenavo, uvanenavo nikukambileni, ine ndi chicheko cha mbelele. 8Onche anyiao anichogolela ndi ankhungu ndi olanda nampho mbelele siwadavechele."9Ine ndi chicheko. Walienche siwalowe kupitila kwanga, siwaokoledwe. Siwalowe mkati ndi kuchoka, nae siwajipezele vakudya. 10Mnkhungu siwaja ingakale kuba, mkumpa , ndikuteketeza, naja ilikuti apate umoyo ndi akaleno tele.11Ine ndi owesa wabwino. Owesa wabwino kuchocha umoyo wake kwa chifuko cha mbelele. 12Mtumiki uyo siwasaukidwa, ndi asati owesa, iyembelele osati chuma chake, siaone agalu amtengo naaja ndi kuwasia ndi kuwatawa achimbelele. 13Ndiagalu amtengo siagwile ndikuwatawanyicha. Kutawa kwachifuko ndi mtumiki kuajiliwa ndi siaganizila mbelele.14Ine owesa wabwino ndi nijiwa ali wanga nao ali wanga anijiwa ine. 15Ambuye anijiwa nane najiwa Ambuye nane niuchocha umoyo wanga kwachiuko cha mbelele. 16Nilimazo mbelele zambili ambazo osati za uzizi achaamene nao. Inifuna kwapeleka, nao saivele sauti yanga ilikuti pakalepo ndi kundi limoji ndi owesa mmoji.17Ichi chiuko ambuye anikonda. Ni uchocha umoyo wanga alafu niukwezancho. 18Palibe wautenga kuchoka kwanga. Nampho niuchocha namwene. Nilinayo mamlaka.''19Mgawanyikoncho udachokela pakati pa Wayahudi kwachifuko cha mau yaya. 20Ambili wao adakamba wali ndi pepo ni ukichaa ndande yanji mumvenchela? 21Wina adakamba, "yamene osati mau yamunthu wachanganyekiwa ndimapepo. Pepo likoza kuchakula maso yakipofu?"22Ndiyapo idaja sikukuu ya kuika waku Kuyerusalemu. 23Idali nyengo yamphepo ndi Yesu wadali wamaendela hekalu katika nyumba ya Selemani. 24Ndiyapo Wayaudi yapoadamzungulila ndikumkambila, "mpaka chakunji siutike mmavuto? Ngati iwe ndi Mkristo tikambile ukweli.25Yesu wadayankha! Natokukambila nampho simuniamini nchito nizichita kwanjina la Ambuye wanga nazo nizishuhudia pamwamba panga. 26Ata chimwecho simuniani kwachifuko anyiimwe ojati mbelele zanga.27Mbelele zanga aivela sauti yanga namjiwa nao au ichata ine. 28Naapacha uzima wa milele siangamiacho kamwe ndi palibe ata mmoji uyo siwanga kule kuchokela mmanja mwanga.29Ambuye wanga yaonipacha achameneo ndi wamkulu kuliko achameneo onche palibe ata mmoji wali ndi uwezo wakuwanyakula kuchokela mmanja mwa Ambuye. 30Ine ndi Ambuye tu mmoji. 31Adatenga myala ili amsinje ncho.32Yesu wadayankha, natokukulangizani nchito za mbili za bwino kuchoka kwa Ambuye kwa nchito ziti kati ya izi mfuna kunisinja myala. 33Wayahudi adamuyankha sitikusinja myala kwa nchito yaliyonche ili yabwino. Nampho kwa kumphemphwa kwa chifuko iwe muntu ujichita kuti Mulungu.34Yesu wadayankha sidalembedwe kupitila lamulo lanu ndidakamba, "anyiimwe ndi miungo?" 35Ikakala adawatana miungu kwa anyiwaja ambao mau la Mulungu lidajela ndi malembo siyakoza kuswedwa. 36Mkamba pamwamba yuja ambaye adamchocha ndi kumtuma kupili kujiko uzalau kwa chifuko ndidakamba, "ine ndi mwana wa Mulungu?"37Ikakala sinichita nchito za ambuye wanga msidaniamini. 38Ata chimwecho ikakala nizichita atangati simuniamini ziaminini nchito nchito ilikuti mkoze kujiwanchi kuzijiwa kuti ambuye wali mkati mwanga nchi iine nili mkati mwa Ambuye. 39Adayesancho kumgwila Yesu nampho wadapita zake kuchokela mmanja mwao.40Yesu wadapita zakencho kung'ambo ya Yordani sehemu ambayo Yohana wadawi wamabatiza hati ndi kukala kumene. 41Wanthu ambili adaja kwa Yesu adaendekela kukamba Yohana kweli siudachite ishara yaliyonchoche, nampho vinthu vonche wadavikamba Yohana pamwamba pa uyu muntu ndi ya uzene. 42Wantu ambili adamwamini Yesu pamene.

Chapter 11

1Basi munthu mmoji jina lake Lazaro wadali odwala. Wadachokela ku Bethania, muji wa Mariamu ni dada wake Martha. 2Wadali ni Marimu yuyuja wadampaka Ambuye mafuta ni kumpangusa myendo yake kwa machichi yake, ambaye m'bale wake Lazaro wadali ni odwala.3Ndeyapo dada anyiyawa adatuma utenga kwa Mpulumusi ni kukamba, "Ambuye, penyani yuja mumkonda wadwala." 4Mpulumusi yapo wadavela wadakamba, "utenda umeneo osati wa kufa, chifuko chake ni kwa ndande ya ufulu wa Mulungu dala kuti mwana wa Mulungu wapate uulu katika umeneo utenda."5Mpulumusi wadamkonda Martha ni dada wake ni Lazaro. 6Yapo wadavela kuti Lazaro ni odwala Mpulumusi wadakala siku ziwili kuendekela pamalo yapowadali. 7Ndo baada ya ili wadakambila opuzila wake, "tieni Kuyahudincho."8Opuzila adamkambila, "amwalimu, Wayahudi amauna kuyesa kukubula myala, nawe ufuna kubwela kumenekoncho?" 9Mpulumusi wadayankha, "saa za usana sizili kumi na mbili? Munthu yapo waenda usana siwakosa kujikwala, ndande wapenya kwa mwanga wa usana."10Ata chimwecho, ikakala waenda usiku, wajikwale kwa ndande mwanga palije mkati mwake." 11Mpulumusi wadakamba vichito ivi, ni baada ya vichito ivi, wadakambila, "bwenji latu Lazaro wagona. Nampho nipita dala kuti nipate kumuucha kuchoka kulitulo."12Nampho opuzila adamkambila, "Ambuye, ngati wagona, siwauke. 13Nthawi ii Mpulumusi wadali wakambilila nkhani za nyia ya Lazaro, nampho anyiio adaganize wakambilila nkhani yogona litulo. 14Ndeyapo Mpulumusi wadakambila uzene, "Lazaro wafa."15Nili ni chisangalalo kwa ajili yanu, kuti sinidalipo kuja dala kuti mpate kukulupalila. Tieni kwa iye." 16Basi, Tomaso watanidwa pacha, wadakambila opuzila achanjake, "nafe tieni pia tikafe pamoji ni Mpulumusi."17Nthawi Mpulumusi yapo wadaja, wadapeza kuti Lazaro tayari watokata mkaburi siku zinai. 18Nayo Bethania idali pafupi ni Yerusalemu ngati kilomita arobaini tano chimwechi. 19Ambili katika Wayahudi adaja kwa Martha ni Mariamu kwachezeche kwa ajili ya m'bale wao. 20Ndekuti Martha yapo wadavela kuti Mpulumusi watokuja, wadapita kupezana naye, nampho Mariamu wadandekela kukala kukomo.21Ndeyapo Martha wadamkambila Mpulumusi, "Ambuye nati mdakakala pano, kaka wanga siwadakafa. 22Ata saino, mjiwa kuti lalilonche mulipemphe kuchoka kwa Mulungu siwakupacheni." 23Mpulumusi wadamkambila, "kaka wako ahyukencho."24Martha wadakambila, "mjiwa kuti wahyuke katika kunyakulidwa siku yotela." 25Mpulumusi wadamkambila, "ine nde kunyakulidwa ni umoyo, iye wanikulupalila, ata chimwecho wakale walama; 26Ni iyewalame ni kunikulupalila ine siwafa. Ukulupalila ili?"27Wadamkambila, "etu, Ambuye nikulupalile kuti iwe ni Mpulumusi, mwana wa Mulungu iye wakuja katika jiko lonche." 28Yapo wadakamba ili, "wadachoka ni kumtana dada wake Mariamu kumphepete, wadakamba, amwalimu ali yapa ni akutane." 29Mariamu yapo wadavela, wadaimuka mwa chisanga ni kupita kwa Mpulumusi.30Nae Mpulumusi wadali wadaji wakali mkati mwa kijiji, wadali wakali pamalo wadapezana ni Martha. 31Ndeyapo Wayahudi wadali ni Mariamu katika nyumba ya anyiwaja adali amamtondoze, yapo adamuona waime chisanga ni kuchoka kubwalo, adamchata, adaganizo kuti wapita kukaburi dala wakalile kumeneko. 32Ndi Mariamu, yapo wadafika paja Mpulumusi wadali wadamuona ni kugwa panchi pamyendo yake ni kumkambilani, "Ambuye ngati mdakali pano, mbale wanga siwadakafa."33Mpulumusi yapo wadamuone walila, ni Wayahudi adaja pamoji ni iye adali amatolila nao, wadadandaula katika mzimu ni kukosa mtendele. 34Wadakamba, "mwamgoneka kuti? Adamkambila, Ambuye, majani mpenye." 35Mpulumusi wadalila.36Nde yapo Wayahudi wadakamba, "penya umo wadamkondola Lazaro!" 37Nampho wina kati ayo adakamba, "osati uyu munthuwadayatambasula maso ya yuja wadali osapenye, wadakoze kumchita uyu munthu wasafa?"38Ndeyapo Mpulumusi wadali wadandaula mumtima mwakencho, wadapita kuli kaburi chapano lidali jenje, ni mwala waikidwa pamwamba pake. 39Mpulumusi wadakamba, "uchocheni mwala." Martha mlongo wake ni Lazaro, iye wafa, wadamkambila Mpulumusi, "Ambuye, kwa muda uno tupi likale laola, kwa ndande watokala chitanda kwa siku zinai." 40Mpulumusi wadamkambila, "ine sinidakukambile kuti ngati ukakulupalila, siuwone ufulu wa Mulungu."41Kwa icho adauchocha mwala. Mpulumusi wadapenya maso yakekumwamba ni kukamba, "atate, niyamika pakuti munivela. 42Nidajiwa kuti munivela nthawi zonche, nampho ni kwa ndande ya gulu ambalo laima kunizugulila kuti nayakamba yaya, dala kuti apate kukulapalila kuti iwe wanituma."43Baada yokamba yaya, wadalila kwa sauti yaikulu, "Lazaro, maja kubwalo!" 44Wakufa wadachoka kubwalo wamangidwa manja ni myendo kwa nchalu zo zikila, ni kumaso kwake kudamangidwa ni kitambaa, " Mpulumusi wadakambila, "Mmasuleni mumsie wajipita."45Ndeyapo Wayahudi ambili anyiyao adaja kwa Mariamu ni kuona Mpulumusi wachichita, adamkulupalila; 46nampho akumoji wao adapita kwa Maarisayo ni kwakambila ivo wavichita Mpulumusi.47Ndipo wakulu akulu anchembe ni Maarisayo adakusanyana pamoji katika pamalo nikukamba, "tichite chiani? Munthu uyu wachita malangizo yambili. 48Ikakala timsia chimwechi iye yoka, onche siamukulupalile, Warumi siaje nikutenga vonche pamalo patu ni jiko latu."49Ata chimwecho, munthu mmoji kati yao, Kayaa wadali wa nchembe wa mkulu chaka chimwecho wadakambila, "simjiwa chalichonche kabisa. 50Simganizila kuti ifai kwa chiuko chanu kuti munthu mmoji iunika kufa kwa chifuko cha wanthu kuliko jiko lonche kufa."51ya wadayakamba kwa chiuko cha mwene, pambuyo pake, pakuti wadali anchembe wamkulu chaka chija, wadalasa kuti Mpulumusi siwafe chiuko cha jiko; 52Niosati kwa jikope toka, kuti Mpulumusi wapate mumuja kwakusenya wanaa Mulungu anyiyao apatuka malo ina ina. 53Kwa icho kuyambila siku limenelo ni kuendekela adapanga umo ampele Mpulumusi.54Mpulumusi wadaendencho padanga kati ya Wayahudi, nampho wadachoka pamenepo ni kupita jiko lili pafupi popanda kanthu katika muji utanidwa Efraimu. 55Basi Pasaka ya Wayahudi idali pafupi, ni ambili amakwela kupita Kuyerusalemu kubwalo kwa muji kabla ya Pasaka dala apate kujichocha chimo achinawene.56Adali kumfunafuna Mpulumusi ni kukamba kila mmoji yapo adali aime mkamba, "inganizila chiani?" 57Muda uno wakulu akulu anchembe ni Maarisayo adali achoche lamulo kuti ikakala mmoji wajiwe Mpulumusi wali, ifunika kuchocha nkhani dala kuti apate kumgwila.

Chapter 12

1Siku sita kabla ya Pasaka, Yesu wadapita Bethania,uko wadali Lazaro, iye uyo wadamuhyusha kuchoka pakati pa akufa. 2Basi adamwandalia chakudya cha unchula kumeneko, ndi Martha wadamtumikila, nyengo imeneyoLazaro wadali mmonchi wa anyiwancha adakhala pa kudya pamonchi ndi Yesu. 3Ndeyapo Mariamu wadatenga latli ya manukato yayoyadakonchedwa kwa nardo yabwino, ya ntengo waukulu, wadampaka Yesu mmyendo, ndi kumpangusa mmyendo kwa chichi lake, nyumba yanchi idanchala mnunkha wa manukato.4Yuda Iskariote, mmonchi wa anyiwancha opuzila wake ambaye ndeuyo siwamuukile Yesu, wadakamba, 5"ndande chiyani manukato yaya sidakagulinchidwa kwa dinari miazi tatundi kwaninkha asauko?" 6Nayo wadakamba yameneyo, osati kwa kuwaonela lisungu osauka, ila ndande wadali mnkhungu; iye nde uyo wadagwila nthumba la hela ndi wadatenga baadhi ya ivovidaikidwa mmenemo ndande yake mwene.7Yesu wadakamba, "msiye waike icho walinacho ndande ya siku ya kuzikidwa kwanga. 8Osauka simkhale nao siku zonche; nampho simnkhala ndi ine siku zonche."9Basi gulu lalikulu la Wayahudiadapata kunchiwa kuti Yesu wali kumeneko, naoncho adancha, osati ndande ya Yesu pe, ila amwone ndi Lazaro uyu Yesu wasamhyusha kuchoka pakati pa akufa. 10Naoncho wakulu anchembe adachita maganizo ili amuimphe Lazaro; 11pakuti ndande yake ambili pakuti pa Wayahudi adapita ndi adamkhulupalila Yesu.12Ndi siku ya kawili yake gulu la likulu lidancha pa sikukuu yapo adavela kuti Yesu wakuncha ku Yerusalemu, 13adatenga nthawi za mitengo ya mitende ndi kuchoka kubwalo kupita kumlandila ndi kubula mapokoso, "Hosana! iye wakuncha kwa nchina la Ambuye, Mfumu wa Israeli."14Yesu wadampata mwana wa punda wadakwela, ngati ndimuncha umoidalembedwa. 15"Usidaopa, mwali wa Sayuni, penya, mumu wako watokuncha, wakwela mwano wa punda."16Opuzila wake siadaelewe vinthu vimenevo pamenepo huti; nampho Yesu yapodatukuzidwa, ndeyapo adakumbuka kuti vinthu ivi wadalembeledwa iye ndi kuti achita vinthu ivi kwake.17Basi lincha gulu la wanthu anyiyawa adalipo pamonchi ndi Yesu nyengo yapo wadamtana Lazaro kuchoka kumakaburi, adashuhudia kwa wina. 18Ndi idali ndande imeneyoncho kuti gulu la wanthu adapita kumlandila ndande adavela kuti wadachita ishara imeneyo. 19Mafarisayo adakmbichana anyiiwo kwa anyiiwo, "penya saino simkhoza kuchita chalichonche, penya, nchiko lapita kwake."20Chipano baadhi ya Wayunani mkali mwa anyiwancha amapita kuabudu pa sikukuu. 21Anyiyawa adamchata Filipo, ambaye wadachaka Bethsaida ya Galilaya, adamphempha adakamba, "Ambuye, ife tukhumbila kumwona Yesu." 22Filipo wadapita wadamkambila Andrea; Andrea ndi Filipo adapita ndi kumkambila Yesu.23Yesu wadaanchibu wadakamba, "saa yafike ndande ya mwana wa Adamu kutukuzidwa. 24Uzene, Uzene, ndikukambilani, chembe ya ngano ngatisiigwa pakati pa nchika ndi kua, inkhala hali imweyo yakhope, ila ikafa, siibale matunda ya mbili."25Iye wakonda umoyo wakesiwautaize, ila iye wauipila umoyo wake pakati pa nchiko ili siwaulamiche hata umoyo wa muyaya. 26Munthu waliyenche wakanitumikila ine, ndi waninchite; nane yapo ndilipo, ndiyapo ndi mtumiki wanga ndiyapo siwakhalepo. Munthu waliyenche wakanitumikila, tate siwamlemekeze.27Chipano mzimu wanga waipidwa; nane nikambe bwanchi? Atate, anilaminche pakati saino? Nampho kwa ndande ii naiikila saino. 28Atate, mulitukuze jina lanu, ndeyapo sauti idaja kuchoka kumwamba ndi kukamba, ndalitukuza nane si ndilitukuzencho. 29Basi gulu lidaima pafupi naye adavela adakamba kuti kuli mtungulu, wina adakamba, "angelo wakamba naye."30Yesu wadajibu ndi kukamba, "sauti ii siidaje ndande ya ine, ila ndande yanu. 31Chipano hukumu ya nchiko ili ilipo; chipano wamkulu wa nchika ili siwatanidwe kubwalo.32Nane ndikainulidwa pamwamba pa nchiko, si ndiaguze onche kwanga." 33Wadayakamba yameneyo ndiwalangizakuti kwa ndisi wa ife.34Gulu lidajibu, "ie tavela pakati pa lamulo kuti Kristo siwadumu paka muyaya. Nawe ukamba bwanchi mwana wa Adamu lazima wainulidwe pamwamba? Uyu mwana wa munthu ndi yani?" 35Basi Yesu wadaakambila, "dangalila likali pamonchi ndi anyiimwe muda kidogo. Mapitani pakuti mlinalo dangalila, ili kuti mdima usidanchakukukhozani iye wapita kumdima siwajiwa uko wapita. 36Mkhakala mkali ndi dangalila likhulupaliloni limenelo ili mpate kukhala wana adangalila." Yesu wadayakamba yameneyo ndi wadapita zake wadajibisa asidamwona.37Ingakhale Yesu wadachita ishara zambili mtundu umeneo pachogolo pao, nampho siadakhulupalile 38ili likamichidwe mau la Isaya olosa , ila wadakamba, "Ambuye ndi yani wadavomela mau yanthu? Ndi chancha la Ambuye wamasulidwa yani?"39Ndo chifukwa cha anyiiwo siadakhulupalile, pakuti Isaya wadakamba ncho, 40"wachita siaponya maso, ndi waichita yolimba mitima yao; asadancha kupenya kwa maso yao ndi kunchiwa kwa mitima yao, ndi kung'anamuka ndi ine kuwalamicha."41Isaya wadakamba mau yameneyo pakuti wadaona uulu wa Yesu ndi wadakamba mau yake. 42Nampho, ata wakulu akulu ambili adamkhulupalila Yesu; nampho ndande ya Maarisayo, siwadavechele ili asidancha kubagulidwa ndi kanisa. 43Adakonda sifa za wanadamu kuliko sifa zichoka kwa Mulungu.44Yesu wadapaza sauti ndi kukamba, "iye wanikhulupaliloa ine, siwanikhulupalila ine pe, ila ndi iye uyowanituma ine, 45ndi uyo waniona ine wamuona ndi uyo wanituma."46Ine nancho ngati dangalila la panchiko ili kila munthu wanikhulupalila ine siwadakhala kumdima. 47Ikakhala munthu waliyonche siwayavenchele mau yanga nampho siwayagwila, ine sindimuhukumu pakuti sindidancho ili ndihukumu nchiko, ila nilaminche nchiko.48Iye wanikana ine ndi uyosiwavomela mau yanga, walinayo wa kumuhukumu; mau ili ilo nakamba nde ilo silimuhukumu siku ya nthela. 49Pakuti ine sindidakambe kwa mtima wangape, ila ndi atate yawo anipeleka, iwo wene anigwiliza yayosindikambe. 50Nane ndinchiwa kuti gwiliza lake ndi la umoyo wa muyaya, basi yameneyo ndikamba ine ngati atate umoadanikambila, ndeumo ndikambila kwanu."

Chapter 13

1Chikondwelelo cha Pasaka chili pafupi, chifukwa Yesu wadajiwa kuti nthawi yake ili pafupi, yochoka pajiko lino kupita kwa atate wake, waakonda wanthu wake adali pajhiko, wadaakonda kupunda. 2Ndi satana watakuikidwa mumtima wa Yuda Iskariote mwana wa Simoni kumupeleka Yesu kwa adani.3Yesu wadajiwa kuti atate wake adakuika vinthu vonche mmanja mwake ndi kuti wachokela kwa Mulungu ndikuti wapita kwa Mulungu. 4Wadauka pa chakudya ndi kuyala chivalo chake pa bwalo, ndipo wadatenga nchalu yopukutila ndi kujimanga mwene. 5Ndipo wadatila maji mbeseni ndikuyamba kuwachukha miendo omphuzila wake ndi kuwapukuta ndi nchalu yopukutila ilo wadajimanga mwene.6Wadapita kwa Simoni Petro, ndi Petro wadamkambila Ambuye, muuna kundichuka mapazi yanga? 7Yesu wadayankha ndikumkambila, sazino icho ndichichita siuchijiwa, nampho siujiwe pambuyo. 8Petro wadamkambila siundichuka mapazi yanga muyaya. Yesu wadayankha ikala ngati sindikuchuka, siukala pamoji ndi ine. 9Simoni Peturo wadamkambila, "Ambuye msandichuka mapazi yangape, ikawe manja ndi mutu wanga."10Yesu wadamkambila, "waliyenche uyo wasamba siwaunika kusambancho ikawe mapazi yake, ndi wakala oyela tupi lake lonche, anyiimwe muli oyera nampho osati mwawonche." 11Pakuti Yesu wadajhiwa uyo siwamng'anamukile nde chifukwa wadakamba, "osati mwaonche muli oyela."12Yesu wapo wamachuka miendo yao ndiyapo wadatenga chivalo chake ndi kukalncho wadakambila bwanji muchijiwa icho ndakuchitilani? 13Munitana ine, "mpuzisi," ndi Ambuye yapa mkamba uzene, mate yake ndimonili. 14Ngati ine ndi mbuye ndi mphuzisi, ndakuchukani miendo yanu, anyaimwe namwe muunika kuwachuka miendo achaanjanu. 15Pakuti ndakupachani chisanzo kuti anyaimwe namwe mchite ngati ine umo ndi machitila kwa anyaimwe.16Ukulupililani, kulupililani, ndikukambilani kapolo siwakula kwa bwana wake, ndi otumidwa siwakala wamkulu kuposa uyo wamutuma. 17Ikakala ujiwa zimenezi, ukachita wadalisidwa. 18Sindikamba kwaanyaimwe mwaonche, ndande ndajhiwa anyiao nda asankha ikapanda ndikamba ili kuti malembo yakhoze kukwanila waliyenche wadya nkate wanga.19Ndikukambilani izi chipano zikali zosaoneke kuti yaposizioneke, mkoze kukulupalila kuti ine ndeine. 20"Kulupalilani ndikukambilani, wanilandila ine wamlandila uyo nda mutuma, ndi uyo wandilandila ine wamulandila uyo wandituma ine."21Nyengo wamakamba izi, wadachauchikha mumtima, wadaona ndi kunena kulupalilani, kulupalilani, ndikukambilani kuti mmoji wanu siwandiguliche. 22Omphuzila wake adapenyana, ndikuzizwa chiukwa cha yani wadakamba.23Adali pa chakudya mmoji wa omphuzila wake wadali pamphepete pa Yesu yuja Yesu wadamukonda kupunda. 24Omphuzila yuja wadali pamphepete pa Yesu wadamuncha, Ambuye ndi yani. 25Yesu wadayankha, ndimene sindisunche nkate ndi kumuninkha, kwaichoyapo wadasuncha nkate, wadamuninkha Yuda mwana wa Simoni Iskariote.26Yesu wadayankha , ndimmene sindisunche nkate ndi kumuninkha, kwaicho yapo wadasuncha nkate, wadamuninkha Yuda mwana wa Simoni Iskariote. 27Pambuyo pa nkate, satana wadamulowa, ndipo Yesu wadamkambila, "icho ufuna kuchichita msanga."28Chipano palije munthu pachakudya paja wadajiwa ndande chiyani Yesu wadakamba mau yaya kwa iye. 29Akumoji wao amajiwa kuti ndande Yuda wamagwira tumba la ndalama, Yesu wadamkambila, gula vinthu ivo tiviuna chiukwa cha chisangalalo, kapena kuti waunika kuchocha chinthu kwa osauka. 30Yuda wakate kulandila nkate, wadatuluka kubwalo msanga ndi udali usiku.31Yapo wadachoka Yuda, Yesu wadakamba, "chipano mwana wa munthu walemekezedwa, ndi Mulungu walemekezedwa mwa iyeyo. 32Mwaiyeyo Mulungu siwalemekezedwe ndi siwamulemekeze mwamsanga. 33Wana wamng'ono ang'ono, ndili namwe panthawe yaiupi, simufunefune, ndi ngati umo ndakambila Ayahudi, uko ndipita, simkhoza kujha chipano ndikukhambilani anyaimwe namwe.34Ndikuninkhani lamulo la chipano, kuti mkondane, ngati ine umo ndidakukondelani anyaimwe, chimwecho anyaimwe nmwe mfunika mkondane anyaimwe kwa anyaimwe. 35Pachifukwa ichi wanthu sajhiwe kuti anyaimwe ndi omphuzira aine, mkakala achikondano."36Simioni Peturo wadamkambila, "Ambuye, mpita kuti?" Yesu wadayankha, "kumalo ukondipita chipano siukhoza kundichata, nampho siundichate pambuyo." 37Petro wadamkambila, "Ambuye, chifukwa chiyani ndisakuchata sazino? Ine sindichoche umoyo wanga ndande yaiwe." 38Yesu wadayankha, "chiukwa chaine siuchoche umoyo wako? Kulupalila, kulupalila ndikukambila tambala wakali osalile siundikane mara katatu."

Chapter 14

1Usidavomeleza umoyo wako kukala pakati pohangaika, umulolela Mulungu munilolele ndiine. 2Pakati panyumba yatate wanga pali ndi nyumba zambili zokala, ngati sidakakala mchimwecho, nidakala nakukambila, pandande nipita kukukonjelani pamalo pandande yako. 3Ngati sinipite ndikukukonjelani malo, sindijejo kukukalibisheni kwanga ili pamalo nili pia namwe mkalepo.4Mujiwa njila pamalo ndipita." 5Tomaso wadamkambila Yesu," Ambuye, sitijiwa kumalo ukoupita, bwa! Tikoza bwanji kuijiwa njila? 6Yesu wadamkambila, "ine nde njila yauzene, ndi umoyo, palibe wakozae kujiwa kwa atate ingakale kupitila kwanga. 7Ngati mudakalijiwa ine, mudakajiwa ndi atate wanga ndipo, kuyambila chopano ndikuendekela mujiwa ndikumuona iye."8ilipo wadamkambila Yesu, "Ambuye tilangize atate, ndichocho sivale yatukwana." 9Yesu adamkambila sindidalipamoji nda nyiimwe kwandawi, yaitali, ndiukuli siundijiwa ine, ilipo? Walionje wamiona ine waona atate, khani yanji ukamba, tulangize atate?10Simuvananavo kuti ine ndimnyumba mwa atate, ndi atate ndi mnyumba mwanga? Mau ndiyakomba kwanu sindikamba padala langa namwene, pambuyo pake, ndi atate yao alama mnyumba mwanga yao achita njito yao. 11Vananavo ine, kuti ndili munyumba mwa atate, ndi atate mnyumba mwanga, ndichocho muamini ine pandande ya njito zanga hasa.12Vananavo, vananavo, ndikukambilani iye wavananavo, ine njito zia nizichitazo, siwazichite nito izi pia, ndi siwachite ata njito zazikulu pandande ndipita kwatate. 13Chilichonche simupembe pajina langa, sindichite pakuti atate akoze kukuzidwa, pakati pamwana. 14Ngati simupembe chindu chilichonje pa jina langa, chimene sindichite.15Ngati simunikonde, simuyakwile malamulo yanga. 16Ndi siniapembe atate, nao sakunikhe ni wakukutangatilani mwina ilikuti wakoze kukala pamoji namwe paufulu, 17Loho yauzene. Jiko silikoza kumlandila iye pandande simumuona, pina kumuji wa iye, ata chochomwe mujiwa iye, pakuti wakala pamoji namwe ndisiwakale mnyumba mwanu.18Sindikusiani mweka, sindibwele kwanu. 19Pandawi yaitali jiko silinionajo, nambo anyiimwe muniona, pandande muniona, pandande nitama, namwe simukale pia. 20Pandawi imeneyo simukale kuti ine ndili mnyumba ya tate, ndikuti anyiimwe muli mnyumba yanga, ndikuti ine nili mnyumba yanu.21Walionje wangwila malamulo yanga ndi kuzichita, nde mmoji uyo wandikonda ine, ndi uyo wanikonda ine siwakondedwe nda atate wanga, ndi sinimkonde ndi sinilangize ine namwene kwake. 22Yuda (apande Iskariote) adamkambila Yesu, "Ambuye, bwa! Ndichiyani chichokela kuti siujilangize umwene kwatu ndiopande pajiko?"23Yesu wadayankha ndikukwambila, "ngati walionje wanikonda, siwaligwile mau langa, atate wanga samkonde, ndisitipite kwake ndi sitichite makazi yatu pamoji naye. 24Walionje uyo siwanikonda ine, siwagwila mau yanga. Mau ilo mulivela opande langa ndipo latate ilo anituma.25Nakamba vindu ivi kwanu, ndawi ni kali ndinikala pamoji namwe. 26Atachocha, oniariji, umoyo wamtendele yao atate siamtume pajina, siwayaluze vindu vonje ndisakuchiteni mukambukile yonje yayo nidayakamba kwanu. 27Mtendele nikunikhani mtendele wanu imwe. Sinikunikhani ii ngati jiko lichochavo nisidachita mitima yanu kukala ndi kuhangaika, ndikuopa.28Mdavela vicha nidakukambilani, nipita zanga, ndisinibwele kwanu! Ngati muda kunikonda ine, mudakakala ndi lahapandande nipita kwatate, pakuti atate ndi wakulu kupita ine. 29Chopano nata kukukambilani popande kuchitika ichi kuti, ndawi sichichitike. mkoze kuvananavo. 30Sindikamba namwe mau yambili, pakuti wamkulu wajiko lino, wabwela iye walibe mbavu pamwamba panga, 31nambo ili kjti jiko lipate kujiwa kuti na konda atate, nichita icho nichita atate anituma ine, ngati umo aninikhila malamulo, imani, nditichoke pamalo pano.

Chapter 15

1Ine ndine mvinyo wauzene ndi atata wanga alimi a mvinyo. 2Ntawi iliyonche mkati mwaine wamenelo silibala chipacho ndi kuliyelecha mtundu wa ntawi lime libala vipacho ndi kulichocha dala kuti likoze kubala kupunda.3Anyiimwe mwakala bwino chifukwa cha utenga umene nidatokukambilani. 4Mkale mkati mwanga nanencho ndikale mkati mwanu ngati ntawi imene sitikoza kubala loka ngati losakala pa mvinyo chi majimoji anyiimwe ngati simkala mkati mwanga.5Ine mvinyo anyiimwe ni ntawi, walimbikicha mkati mwanga nanencho ndili mkati mwake muntu mmeneyo wabara vipacho vambili pakati popande ine sipanga chitidwe chinthu chilichonche. 6Ikakala muntu waliyenche siwakala mkati mwanga siwatanidwe ngati ntawi ndi kuuma, wanthu alombekane ntawi zonche kutaya pamalo ndi kutelatu. 7Ngati simkale chikalileje mkati mwaine ndi ngati mau yanga siyakale chikalileje mkati mwanu pemphani chilichoche simdiiune namwencho sinichitidwile.8Paili tata wanga walemekezedwa kuti mbala vipacho vambili ndi kuti oyaluzidwe wanga. 9Ngati simuyagwile malambo yanga simkale pa chikondi changa ngati umo ndidagwirila malamulo ya atata wanga ndi kukala pakati pa chikondi chake.10Ngati simuyagwile malambo yanga, simkale pa chikondi changa ngati umo ndidagwirila malamulo ya atata wanga ndi kukala pakati pa chikondi chake. 11Nde kamba nkani izi kwa anyaimwe dala kuti chisangalalo changa chikale mkati mwanu ndidela kuti chisangalalo chano chichitika pauzene.12Ili nde lamulo langa kuti mjikondeni mwachinawene kwa mwachinawene ngati ine umo nde kukudelani. 13Palije muntu wali ndi chikondi chachikulu kupunda ichi kuti wachoche kulama kwake chiuko cha mabwenji lake.14Anyaimwe mabwenjo langa ngati simchite yamene ndi kukambilani. 15Sindikutanani akaporo pakuti kaporo siwachijiwa icho wachichita wamkuru wake nakutanani anyaimwe mabwenji chifukwa chakujiwichani nkhani zonche ndezivela kuchokela kwa atate.16Simdeni sankule ine ikapanda ine na kusankhulani anyiimwe ndi kukuikani kuti m'bale vipacho ndi chipacho chano nikoze kukala. Ichi chilichimwe dala kuti chilichonche mpempha kwa atate kupitila mjina laine siakupacheni. 17Nkani izo ndi kupachani kuti mjikondana aliyenche ndi mujake.18Ngati jiko silikuipileni mjiwe kuti mdandiipila ine pambuyo simdaipidwe anyiimwe. 19Ngati mkadakala ajiko jiko likadakukondani ngati akumo nampho pakuti anyiimwe osati ajiko ndi chiuko ndidakusankhulani kuchokela mjiko nde chifukwa jiko likuipilani.20Kumbukilani mau ndidakukambilani kaporoi osati wamkuru kupunda wamkuru wake ngati adandivuticha ine ndi anyaimwe simvutichdwe ngati adagwira mau langa akadaligwila kwa anyaimwe. 21Siakuchitileni nkanizi zonche chifuko cha jina langa chifuko samjiwa mmene wandituma. 22Ngati sindideka bwela ndikukambilani siakadachita machimo nampho chapano alibe chokamba chifuko cha machimo yao.23Wandipita ine wanipita tata wanga. 24Ngati sindichita nchito mkati mwao ikakala imene palije mmoji waichita akada kala alibe chimo nampo chapano achita yonche yawili aona ndi andipila ine ndi atate wanga. 25Ichi chachokela kuti mau ligwirizila limene lalembedwa pa lamulo lao: "andiipila ine palije ndande"26Ntawi mtondoza wafike mmene sindimtume kwanu kuchokela kwa atata wanga uyu ndiye mtima wa zene mmene wachokela. 27Anyaimwe namwencho mundu jililila chifuko mdali nane chiyambile mmayambo.

Chapter 16

1Nakambila vichito ivi kuti msadakoza kuipichidwa. 2Siakuchocheni kubwalo kwa masinagogi, zene nthawi ikujha iyo kila uyosiwakupheni siwaganizile kuti wachita nchito ya bwino kwa ndande ya Mulungu.3Siakuchitileni vichito ivi kwa ndande siamjhiwa tate penancho siaijhiwa ine. 4Nakambila vichito ivi kuti nyengo ukafika wayaya kuchokela, simkoze kuyakumbukila ndi ntundu umo wakukambilani mkoze anyiiwo. Sinidakukambileni kukuza vichito ivi kuyambila mmayambo kwa ndande nidali pamojhi namwe.5Ingakale chipano nipita kwa yujha wadanituma, nampho palibe mwa anyiimwe uyowanifuncha, "upita kuti?" 6Kwa ndande nanena mau yaya kwa anyiimwe; chisoni chajhala mmitima mwanu. 7Ata chimwecho, nikukambileni zene: ni bwino kwa anyiimwe nikachoka. Kwa mate ngatisinichoka otondoza siwajha kwanu, nampho nikapita sinimtume kwanu.8Wakala mmeneyo otondoza kuchimikizila jhiko kulingana ndi machimo kulingana ndi malinga ndi kulingana ndi malamulo. 9Kulingana ndi machimoo kwa ndande siadanikukupalile ine, 10kulingana ndi malinga kwa ndande nipita kwa atate, ndi simnionancho. 11Ndi kulingana ndi malamulo kwa ndande wamkulu wa jhiko lino walamulidwa.12Nilinayo yambili ya kukukambila, nampho simzindikila chipano. 13Nampho, iye mzimu wa zene, wakajha, siwakuchogoleleni muzene yonche, pakuti siwakambancho kwa chifuko chake mwene; nampho waliyenche siwayavele, siwayanene yochitika yameneyo, ndi kuyachinikiza kwa anyiimwe yochitika yayo siyajhe. 14Iye siwanikuze ine, kwa ndande siwayatenge yochitika yanga ndi kulalikila kwanu.15Vindhu vonche alinavo atate ndi vayine, kwa icho, ninena kuti mzimu siutenge vochita vanga ndi kuyachimikiza kwanu. 16Ikali ntawi yaifupi simunionancho, ndi pambuyo pa ntawi ya iupi, simunionancho.17Akumojhi wa opunzila wake adamunchana, "ndichiyani ichowatikambila," ntawi yaifupi simunionancho, ndi , ndipo ntawi ya ifupi simunione, "ndi kwa ndande nipita kwa atate?" 18Kwaicho adanena, "ndi chindhu chanji ichowanena, ikali ntawi yaiupi?" Sitijiwa umowanenela.19Yesu wadanena kuti adakumbila kumuncha ndiiye adakambila, "mjhifuncha mwachinawene kukuza ili, umowanenela ikali ntawi yaifupi simunionencho, ndi pambuyo pa ntawi ya iupi simunione?" 20Zene zene, nikukambilani, simulile haikudandaula, nampho jhiko silikondwele, simkale ndi chisoni nampho chisoni chanu siching'anamukile kukala chimwemwe. 21Wamkazi wakala ndi chisoni nyengo yapowakala ndi vopweteka kwa ndande nyengo ya kujhimasula yoika, nampho yapowajhimasula mwana, siwakumbukilancho vopweteka kwa ndande ya chimwemwe chake kuti mwana wabadwa pajhiko.22Ninyi pia mna huzuni sasa, lakini nitawaona tena; na mioyo yenu itafurahi na hakuna atakayeweza kuiondoa furaha yenu. 23Siku hiyo hamtaniuliza maswali. Amin, Amin, nawaambia, Mkiomba lolote kwa Baba, atawapa kwa jina langu. 24Mpaka sasa hamjaomba lolote kwa jina langu; ombeni, nanyi mtapokea ili kwamba furaha yenu ikamilike.25Nakamba nsi anyiimwe kwa mkambo osajhiwike, nampho nyengo ikujha yapo sinikamba kwa mkambo osajhiwike nampho pambuyo pake sinikukambileni poyelayela kukuza Atate.26Siku limenelo simpemphe kwa jhina langa, ndi sinikukambilani kuti sinipemphe kwa atate kwa chiuko chanu; 27Pakuti atate wene akukondani kwa ndande mnikonda ine ndi kwandande mnikulupalila kuti nachoka kwa atate. 28Nidachoka kwa atate ndi najha pajhiko penancho, nichoka pajhiko ndi nipita kwa atate.''29Opunzila wake adamkambila, upenya, chipano ukamba poyelayela ndi siuchita kwa vindapi. 30Chipano tijhiwa kuti ujhiwa vichito vonche ndi siufuna mundhu waliyenche akuunche mauncho kwa ndande iyi tiikulupilila kuti uchoka kwa mulungu. 31Yesu asawayankha, "chipano mwakulupalila?"32Penyani, nyengo ikujha yetu ndi chiichimichimi yaika, pamene simjhisonghaniche kila mmoji kwake kwake simunisiye namwene. Nampho sinilindeka kwa ndande atate alipamojhi ndiine. 33Nikukambilani vichito ivi kuti mkati mwanga mkale ndi mtendele. Pajhiko mli ndi mavuto, nampho jipacheni mtima, nalikoza.

Chapter 17

1Yesu wadayakamba mau yaya, ndipo wadapenya maso yake kumwamba ndikukamba, "atate nthawi yawandikila, mkuzikeni mwana wanu kuti naye mwana wakuzikani imwe. 2Ngati muja mwampachila malamulo pamwamba pa vinthu vonche vili ndi tupi waapacha moyo wa muyaya onche yao mwampacha."3UUnde moyo wa muyaya kuti akujiwe iwe Mulungu wa zene ndi weka ndi iye mwamtuma Yesu Kristo. 4Nidakukuzikana pano pajiko la panchi ndi kuikwanilicha nchito mdanipacha niichite. 5Chipano atate mnikuzika ine ndi mwawene kwakuyera kuja nidalinako pamoji ndi imwe likali kulengedwa jiko la panchi.6Nidalivunukula jina lanu kwa wanthu mdanipacha pano pajiko la panchi, adali wanthu wanu nampho mdanipacha ine nao aligwila mau lanu. 7Chipano ajiwa kuti kila chinthu mdanipacha ine ine chichoka kwa imwe. 8Kwa mau yaja mdanipacha ine natoapacha anyiiwo mau yaja, adayalandila ndi zene adajiwe kuti ine nachoka kwanu ndi kukulupilila kuti imwe nde mwanituma.9Naapemphela anyiiwo sinilipemphela jiko la panchi nampho waja mwanipacha pakuti anyiiwo wanu. 10Vinthu vonche vaine vanu ndi ivo mulinavo imwe vanga, nane nikuzika kupitila vimenevo. 11Ine nilijemo mjiko la panchi, anyiiwo alimo mjiko la panchi ine chapano nikuja kwanu, atate oyera pa jina lija mdanipacha, mwasunge akale limoji ngati umo tili ife limoji .12Yapo nidali nao nidaasunga pa jina mdanipacha, nidaasunga siwadasowe ata mmoji ingakale mwana osokelela kuti malembo yakwanile. 13Nikuja kwanu chipano nampho nikamba yaya pa jiko la panchi kuti chimwemwe changa chikwanilichidwe mkati mwao. 14Naapacha mau lanu, jiko la panchi laapila ndande anyiiwo osati ajiko la panchi ngati umo nili ine osati wa jiko la panchi.15Ine sinipempha kuti mwachochepa jiko la panchi nampho mwasunge ndi satana. 16Anyiiwo osati ajiko la panchi ngati umo nili ine osati wa jiko la panchi. 17Mwayelese mwa uzene uja maulanu nde uzene.18Ngati muja mudanituma ine nijiko la panchi nane nidaatuma nijiko la panchi. 19Pandande ya anyiiwo najiyelesa namwene kuti nao ayelesedwe mu uzene.20Osati anyiiwope naapemphelo nampho na anyiwajha saanikhulupalile kupitila mau yao. 21Kuti nao akale limoji ngati imwe atate, umo muli mkati mwanga ndiine mkati mwanu, naoncho akale mkati mwa mwatu, kuti jiko la panchi livomela imwe nde mwanituma.22Nane kuyera kuja mwanipacha naapacha anyiiwo kuti akale limoji ngati ife umo tili limoji. 23Ine mkati mwao ndi imwe mkati mwanga, kuti akwanilisidwe mu limoji kuti jiko la panchi lijiwe imwe nde mwanituma, mdaakonda anyiiwo ngati umo mdanikonda ine.24Atate yao mdanipacha niuna akale pamoji ndi ine paliponche yapo nili akoze kupenya kuyera kumene mwanipacha pakuti mdanikonda jiko la panchi likali kulengedwa.25Atate a malinga jiko la panchi silidakujiweni,nampho ine nikujiwani ndi ajiwa kuti mudanituma. 26Nidalichita jina lanu lijiwike kwa anyiiwo ndi sinilichite lijiwike kuti mwa chikondi chija mudanikondela ine chikoze kukala mkati mwao.

Chapter 18

1Pambuyo pa Yesu kukamba mau yaya, wadachoka ndi opuzila wake kupita kubonde la Kidroni, uko kudali ndi bustani, uko iye ndi opuzila wake adalowa mkati mwake. 2Chipano yujha Yuda, yujha wadauna kumgulicha, nae wadayajhiwa malo malo yajha, pakuti Yesu wamapita malo yajha nyengo ndi nyengo wali ndi opuzila wake. 3Nayo Yuda, pamalo polipata gulu la askari ndi maoisa kuchokela kwa wakulu akulu a makuhani, adajha ali ndi nyali, khulunzi ndi4Nae Yesu, nyengo niwajhiwa kila chinthu icho chimachitika pakati pake, wadaatulukila pachogolo ndi kwaauncha, "yani mumfunafuna?" 5Nao adamuyankha, "Yesu Mnazareti." Yesu wadaakambila, "nde ine" nae Yuda uyowadamgulicha, wadaima pamojhi ndi anyiwajha askari.6Kwa chimwecho yapo wadaakambila, "Nde Ine" adabwela mmbuyo ndi kugwa panchi. 7Nampho wadaafunchancho, "Yesu Mnazareth."8Yesu wadayankha, "nathokukambilani kuti nde ine pano; kwa chimwecho ngati munifunafuna ine, asieni anyiyawa wina ajhipita." 9Yaya yadali n'chimwecho, kuti lijha mau litimilike; pajha wadakamba, "pakati pa wajha udanipacha, sinidamsowese hata mmojhi"10Nde Simoni Petro, uyo wadali ndi upanga waufuta ndi kumdulasikio la kwene mtumiki wa kuhani wamkulu. Ndi jhina lake mtumiki yujha lidali Malko. 11Yesu wadamkambila Petro, "bweza upanga wako muala yake. Ndande yanji sinidachimwela chikombe chijha anipacha Atate."12Basi lijha gulu la askari ndi jemedari, ndi atumiki wa Ayahudi, adamgwila Yesu ndi kummanga. 13Nao adamchogoza huti mbaka kwa Anasi, ndande iye wadali mkazake wa KAyaa, iye nde wadali kuhani wamkulu kwa chaka chimenecho. 14Chapano Kayafa nde uyo wadaapacha, mlandu Ayahudi kuti idafunika munthu mmojhi wafe kwa chifuko cha wanthu.15Chapano Kayafa nde uyo wadaapacha, mlandu Ayahudi kuti idafunika munthu mmojhi wafe kwa chifuko cha wanthu. Simoni Petro wadamchata Yesu, ndi n'chimwecho opuzila wina, ndi yujha opuzila wamajhiwike na kwa kuhani wamkulu, nae wadalowa pamojhi ndi Yesu pakati pa behewa la kuhani wa mkulu. 16Nampho Petro wadaima kubwalo kwa chicheko chipano yujha opuzila uyowamajhiwikana kwa kuhani wamkulu, wadachoka kubwalo wadapita kukambana ndi yujha wamkazi mtumiki uyo wadaliolilindila chicheko ndi kumlovya Petro mkati.17Basi yujha mtumiki uyowadali openyelela chicheko, wadamkambila Petro, "iwe si mmojhi wa opuzila a uyu munthu?" Nae wadakamba, "osati ine." 18Ndi anyiwajha atumiki ndi wakulu akulu adaima pamalo pajha, adasonkha moto kwa chifuko kudali mphepo, ndi chimwecho amaota moto kuti apate mfundila. Nae Petro wadali nao, wamaota moto wadaima.19Kuhani wamkulu wadamfuncha Yesu pakati pa opuzila wake ndi mayaluzo yake. 20Yesu wadamuyankha, "nalikambila waziwazi jhiko; ine nidayalu nyengo ndi nyingo mmasinagogi ndi mmahekalu mmalo umo Ayahudi akomana. Nane sinidakambe lalilonche pakati pa chisisi. 21Ndande yanji mudanifuncha? Afuncheni anyiyao adanivechela pakati pa chijha nidachikamba. Anyiyawa wanthu ajhiwa vinthu vijha nidavikamba."22Yesu yapowadathokamba yameneyo, mmojhi wa wamkulu wa nchembe uyo wadaima wadambula Yesu kwa jhanja lake ndi kukamba, "bwanji chimwecho nde umo ufunika kumuyankha wamkulu wa makuhani?" 23Nae Yesu wadayankha, ngati nakamba chinthu chalichonche choipa basi mmboni kwa chifuko cha volakwa, ndi ngati nayankha bwino kwa chiyani kunibula? 24Ndipo Anasi yapowadampeleka Yesu kwa Kayafa kuhani wamkulu wadali wamangidwa.25Chipano Simoni Petro wadaima wamaotha moto mwene. Alafu anyiwajha wanthu adamkambila, "bwanji iwe nawe si mmojhi wa opuzila wake?" Wadakana wadakamba, "opande ine." 26Mmojhi wa atumiki wa makuhani wa kulu, uyo wadali m'balewa yujha wammuna uyo wadamdula sikio Petro, wadakamba, "bwanji iwe nidakuona nae kujha kubustani?" 27Petro wadakanancho, ndi mala tambala wadalila.28Ndipo adamtenga Yesu kuchokela kwa Kayafa mbaka Kupraitorio. Idali umawa mawa anyaio achinawene sadalowemo mprairio ili saadakwiichidwa ndi kuidya Pasaka. 29Kwa chimwecho Pilato wadaapitila wadakamba, "ni mlandu wanji uwoumkhuza munthu uyu?" 30Adamuyankha ndi kumkambila, "ngati munthu uyu siwadakakhala ochita volakwa, sitidakampeleka kwako."31Pilato wadaakambila, "mtengeni anyiimwe mwachinawene, mukamlamule kulingana ndi thauko lanu." Nao Ayahudi adamkambila, "thauko silitilamula ife kumpa munthu waliyonche." 32Adakamba yaya kuti mau la Yesu lienele, mau ilo wadatholikamba pakati pa ntundu wa nyia yake.33Basi Pilato wadalowancho Mpraitorio wadamtana Yesu, wadamkambila, "bwanji iweni mumu wa Ayahudi?" 34Yesu wadamuyankha, "bwanji iwe unifuncha funcho ili chifuko ufuna kujhiwa kapena kwa chifuko wina akutuma kuti unifunche ine?" 35Nae Pilato wadamuyankha, "Si Muyahudi kapena osati?" Khamu lako la kuhani wamkulu nde akupeleka kwanga, iwe wachita chiyani?36Yesu wadayankha, "ufumu wanga osati wa jhiko lino, ngati ufumu wanga udakakhala ndi malo pakati pa jhiko lino atumiki wanga adakaniyambanilanna kuti nisadachochedwa kwa Ayahudi. Kwa chazene ufumu wanga siuchokela pano," basi 37Pilato wadamkambila, "bwanji iwe basi ni mfumu?" Yesu wadayankha, "iwe nde umo ukambila kuti ine ni mfumu, kwa chifuko ichi ine najha pajhiko kuti nikhale mmboni wa ujha uzene. Waliyonche wali wa ujha uzene wayavechela mau yanga."38Pilato wadamkambila, "zene ni chiyani?" Nae yapo wadathomaliza kukamba yaya wadapita kwa Ayahudi ndi kwakambila, "siniona lalilonche pakati pakati pamunthu uyu. 39Anyaimwe muli ndi utamaduni uwo unichita nimmasulile omangidwa mmojhi nyengo ya Pasaka, bwanji mfuna nimmasulile mfumu wa Ayahudi" 40Ndipo adachita mapokoso naakamba, "opande uyu timasulileni Baraba," nae Baraba wadali mnkhungu.

Chapter 19

1Panja Pilato wadamtenga Yesu ni kumtyapa. 2Anyiwajha waaskari adavilinga minga ndikukonja taji, adaiika pamwamba pamunthu ya Yesu nikumvalicha chalu za rangi ya zambalau. 3Adamchata ndikukamba, "iwe mfalme wa Yahudi!" nikumbula ni manja yao.4Panja Pilato wadanjoka kubwalo, ndi kuwakambila wanthu, "penyani nipelekelani uyu munthu kwanu ili mnjhiwe kunti ine sidaiyone hatiya yaliyonche mkati mwake." 5Kwachimwecho Yesu wadachoka kubwalo, wadavala chisoti cha minga ndi chalu za zambalau. Ndi panja Pilato wadakambila, "penyani munthu uyu yapa!" 6Kwachimwecho nyengo kuhani wamkulu ndiwakulu akulu yapo wadamuona Yesu, adapiga kelele adakamba, "msulubisheni, msulubisheni" Pilato adawakambila, "mtengeni anyiimwe mwanjinawene mkamsulubishe, pakuti ine sini iyona ndande mkati mwake."7Wayahudi adamyankha Pilato, "ife tulinayo sheria ndi kwesheria imeneyo ifunika kufa kwandande iye wadanjitita kunti mwana wa Mulungu." 8Pilato panja wadavela mau yaya wadazidi kuusopa. 9Wadalowa Praitorio ndikumkambila Yesu, iwe uchoka kuti? Atamchimwecho Yesu swadayange.10Lakini Pilato, bwa iwe siukamba ndi ine? Bwa iwe siunchiwa kuti ine nili ni mamulaka ya kukuchakulila ni kukusulubisha? 11Yesu wadayankha, "sudakakala ndi mphavu zidi yanga ngati sudakapachidwa kuchoka kumwamba. KWachimwecho, munthu wanichoncha kwako wali ni zambi yaiukulu."12Kuchokana yanko ili, Pilato wadafuna kumsia huru, nampho Wayahudi wadapinga kelele wadakamba, "ngati sumsie huru basi iwe osati mbwenji wa Kaisari; Kila wnjitita kuti mfalme kukamba mmbuyo Kaisari." 13Pilato yapo yadavela mau yaya, wadampeleka Yesu kubwalo kumkalicha pampando wa hukumu pamalo paja pajulikana ngati masakafu, nampho kwa Kiebrania, Gabatha.14Siku ya maandilizi ya Pasaka yapoudafika ndiyani ya saa sita Pilato wadakambila Wayahudi, penyani Mflume wanu uyu yapa. 15Adapiga makelele, mchocheni mchocheni, msulubisheni, Pilato wadakambila, "ndi msulibishe mfalme wanu?" Nayo kuhani wamkulu wadayankha "ife tilibe mfalme ingakale Kaisari." 16Ndeyapo Pilato wadamchocha Yesu kwao ili watesedwe.17Nao adamtenga Yesu. NAe wadachoka hali wautenga msalaba wake mwene mpaka kueneo lidanidwa fuvu la mutu, ndi Kihebrania litanidwa Golgotha. 18Ndiyapo adamsulubisha Yesu pamojhi nae wachimuna awili, mmojhi upande uu ndimwina upande wina, ndi Yesu pakatikati.19Potela Pilato wadalemba alama ndikuiika pamwamba pa msaba pamenepo padalembedwa; YESU MNARETH, MFALME WA WAYAHUDI. 20Ambili wa Wayahudi adaisoma alama ija kwani pamalo paja adamsulubisha Yesu padali pafupi ndi muji. Alama ija idalembedwa kwa Kiebrania kwa Kirumi ndi kwa Kiyunani.21Potela wakulu wa makuhani wa Mayahudi adamkambila Pilato, "si udalemba, Mfalme wa Wayahudi, mpha iye wadakamba ine ndi mfalme wa Wayahudi." 22Nae Pilato wadayankha, "yayonayalemba na yalemba."23Pambuyo askari kumsulibisha Yesu, adatenga vivalo vake ndi kuyagawa mafungu, yanai, kila askari fungu limoji,kwa chimwecho ndi kanzu, chipano lija kanzu, silidali losokedwa nampho lidali lofumidwa lonche kuchola kumwamba. 24Potela adakambichana achinawene kwa achinawene, "sitidaling'amba ila tilitimbile kura ili tione siikale ya yani." Ilimenelo lidachoke lija lembo litimie ilo lakambidwa adagawana nchalu zanga ndi "valo langa adalipigira kura."25Waaskari wadatenda mama yaya. Mama wake Yesu ndi Mariamu mke wa Kleopa ndi Mariamu Magdalena. 26Yesu yapowadamuona mama wake pamoji ndi yujha opuzila uyowadamkonda adaima pafupi wadamkambila mama wake wamkazi kapena taona, mwana wako uyu yapa. 27Potela wadamkambila "yuja opuzila penya uyoyapa mama wako." Chokela chipano uyo yuja opuzila wadamtenga kupita kukomo kwake.28Pambuyo pa ili. Hali Yesu adajiwa kutiyonche yatokala kuta ili kuyatimiza malembo wadakamba, "niona lujo." 29Chombo icho chida likujala siki chidali chaikidwa paja kwachimwecho adiika sifongo iyo idajala siki pamwamba pa ufito wa hisopo adamwikila mkamwa mwake. 30Nae Yesu yapowadailawa imeneyo, Wadakamba, "yotela potela wadakulamicha mutu wake, wadaikabidhi roho yake."31Kwa pakuti idali ndi nyengo ya maandalio ndi kwa ajili matupi siyadafunike kukala pamwamba pa msalaba nyengo ya sabato, pakuti sabato idali nthawi ya bwino, Wayahudi adamphempha Pilato kuti myendo yao waja yaowadali asulubishidwa ityake, ndikuti matupi yao ichichidwe. 32Ndipo asikari yapoadaja ndikutyola myendo ya munthu oyamba ndi akawili uyowadali amsulubisha palimoji ndi Yesu. 33Yapo adampeza Yesu, adampeza tayali wadali watokufa kwa chimwecho siadamtyole myendo yake.34Ata chimwecho, mmoji wa askari adam'bucha Yesu mntiti kwa mkuti, ndi mara yadachoka maji ndi mwazi. 35Nae wadapenya wachocha ushuhuda, ndi ushuhuda wake, ndi wauzene iyo wajiwa kuti ichowachikamba ndi cha uzene ili namwe mvanenavo.36Vinthu ivi ili likwanile lijalakambidwa lipate kukwanila, "palibe ata wake mmoji uosiotyole." 37Tena lembo lina likamba, "siampenyele iye uyoamtosa."38Pambuyo pa vinthu ivi Yusufu wa Arithamaya kwachimwecho wadali opuzila wa Yesu. Nampho kwa kwa siri ya kuwaopa Wayahudi, adamphempha Pilato kuti walitenge tupi la Yesu. Nayo Pilato wadampacha ramulo. Kwa chimwecho Yusufu wadaja kuchocha tupi la Yesu. 39Nayo Nikodemo ambapo pamenepo poyamba wadamchata Yesu usiku nayo wadaja, iyo wadampeleka mchanganyiko wa manemane ndi udi, yapate kulemela ratili mia moja.40Kwachimwecho adalitenga tupi la Yesu adauvilinga msanda ya kitani ndi pamoji ndi yaja malashi ngati umoidali kawaida ya Wayahudi nyengo yakuzika. 41Pamalo wadani Yesu adamsulibisha padali ndi bustani, mkati ya ija bustani mdali ndi kabuli la mpya ambalo padalibe muntu wadawahi kumzika mmenemo. 42Basi pakuti idali siku ya maandalio kwa Yahudi ndikwa chija likabuli lidali karibu, basi adamgoneka Yesu mkati mwake.

Chapter 20

1Chisanga siku loyamba la juma, kukali kuli mdima. Mariamu Magdalena wadaja kukaburi, wadauona uja mwala wachochedwa pakaburi. 2Kwa icho wadatamanga liwilo kupita kwa Simoni Petro ni kwa yuja opuzila mwina ambae Mpulumusi wadamkonda, badae wakamkambila, "amtenga Ambuye pakaburi, nae sitijiwa uko amng'oneka."3Nampho Petro ni yujha opuzila mwina adachoka, kupita kukaburi. 4Onche adatamanga liwilo kwa pamoji, yuja opuzila mwina wadatamanga kwa chisanga kumshinda Petro nikufika kukaburi oyambila. 5Wadaima ni pambuyo kuzuzumila pakaburi, wadaione ija nchalu yoela yagone, nampho wadalowe mkati.6NAmpho Simoni Petro nae wadaika ni kulowa mkati mwa kaburi wadaiona ija nchalu yoela yagona paja 7nichija chitambaa chidali kumutu wake siidagone pamoji ni zija nchalu zoela (sanda) bali idali yagona pamphepete payoka.8Ndipo yuja mwina nae wadalowa mkati mwa kaburi, wadapenya ni kukulupalila. 9Pakuti hadi nthawi imeneyo akali adayajiwe malembo kuti idaunika Mpulumusi wahyuke ncho kwa akufa. 10Pambuyo opuzila adapitancho kunyumba yao.11Ata nchimwecho, Mariamu wadali wa wakali waima pakaburi walila, yapo wadali wakali kuendekela wadaima pambuyo wadapenya mkaburi. 12Wadaona angelo awili ali ni nkhope yoela akala mmoji kumutu ni mwina kumyendo pamalo yapo Mpulumusi wadali wagone. 13Nao adamkambila, "wamkazi, ndande chiani ulila?" Nae wadamkambila, "ni ndande amtenga Ambuye wanga, nane sinijiwa uko amuika."14Yapo wadatokamba yameneyo, wadang'anamuka ni kumuona Mpulumusi wangoina. Nampho wadamjiwe kuti ngati iye wadali Mpulumusi. 15Naye Mpulumusi wadamkambila, "mama, ndande chiani mlila? Mumfunafuna yani?" Nao uku akaganiza kuti ni openyelela bustani adamkambila, "Ambuye, ngati ni imwe mwamtenga, nikambileni uko mwamuika, nane nikamtenga."16Mpulumusi wadakambila, "Mariamu" naye wadang'anamuka mwene nikwakambila kwa Kiaramu, "Raboni," ili ni kukamba, "Opuzila." 17Mpulumusi wadamkambila, "siudanigusa, pakuti nikali osakwele kupita kwa atate, bali upite kwa achabale wanga ukakambile kuti nikwele kupita kwa atata wangu ambao anyiimwe atata wanu. Mulungu wanga ni Mulungu wanu." 18Mariamu Magdalena wadaja kwakambila opuzila, "niona Ambuye," nikuti amkambila mambo yaya.19Ni yapo idali ujulo, siku limenelo, siku loyamba la juma, vicheko vamangidwa pamalo opuzila yapo adali kwa kwaopa Wayahudi, Mpulumusi wadaja ni kuima pakati pakati pao nikwakambila, "mtendele ukale kwa anyiimwe." 20Yapo wadatokamba yameneyo wadalangiza manja yake ni nthili yake. Nao opuzila yapo adamuona Ambuye adasekelela.21Pambuyo Mpulumusi wadakambilancho, "mtendele ukale ni anyiimwe, ngati muja baba adanituma ine, chimwecho ine nane nikutumani anyiimwe." 22Mpulumusi yapo wadatokamba yameneyo, wadachelela wadakambila, "landilani Mzimu oyela. 23Waliyonche umlekelele chino, alekeleledwa, ni anyiwaja mwamangila amangilidwa."24Tomaso, mmoji wa anyiwaja kumi ni awili, watanidwa, Dismasi, siwadali ni opuzila achanjake yapo wadaja. 25Anyiwaja opuzila wina adamkambila pambuyo, "taona Ambuye." Nae wadakambila, "ngati siniona alama za misumari katika manja yake, ni kuika vyala vanga kuzimenezo alama, ni pia kuika janja lanja kunthiti yake sinikulupalila."26Baada ya siku nane opuzila adali kuchumbancho, nae Thomaso wadali pamoji nao. Nthawi vicheko yapo vidali vachekedwa Mpulumusi wadaima pakatikati pao, ni wadakamba, "mtendele ukale namwe." 27Pambuyo wadamkambila Thomaso, janancho chala chako ni upenye manja yanga, janayo pano manja yako ni uike mthili mwanga, wala siudakala osakulupalile, ila okulupalila.28Naye Thomaso wadayankha ni kumkambila, "Ambuye wanga ni Mulungu wanga." 29Mpulumusi wadamkambila, pakuti waniona wakulupalila, adaasidwa anyiyao akulupalila popande kupenya.30Pambuyo Mpulumusi wadaita langizo lalikulu pamaso pa opuzila, izo zidawahi kulembedwa katika chikala kala ichi. 31Nampho izi zalembedwa dala kuti mkoze kukulupalila kuti Mpulumusi. Mwana wa Mulungu, nikuti pokulupalilapo mkate ni umoyo kwa jina lake.

Chapter 21

1Baada ya vinthu vimenevo Yesu wadajilangizancho kwa opuzila pakati pa nyanja ya Tiberia, mchimwecho ndeumo wadajilangiza mwene. 2Simoni Petro wadali pamonchi ndi Thomaso wadanidwa Didimasi, Nathanieli wa Kana ya Galilaya wana a Zebedayo ndi opuzila wina awili a Yesu. 3Simoni Petro wadakambila, "ine nipita kuvua nchomba. Nao adamkambila, "ife nafe situpite ndi iwe." Adapita ndi kulowa mpati nampho usiku umeneo wonche siadapate chalichonche.4Ndi umawa yapo kudacha, Yesu wadaima mphepete, Nao opuzila siadajiwe kuti wadali Yesu. 5Ndeyapo Yesu wadaakambila, "anyamata mli ndi chalichonche chakudya?" Nao adajibu, "palibe." 6Wadaakambila, "nchichani chilopa bendeka la kwene la bwato, namwe simpate kidogo." Kwaiyo adachicha chilepa naoncho siadakhoze kuguzancho ndande ya kuchuluka kwa nchomba.7Basi yuncha opuzila ambayo Yesu wamkonda wamkambila Petro, "Ndi Ambuye." Naye Simoni Patro yapo wadavela kuti ndi Ambuye, wadajimanga nchalu yake (pakuti siwadalivale bwino), ndeyapo wadajitaya myancha. 8Anyiwancha opuzila wina adancha m'bwato (pakuti siadali patari ndi pamtunda, idali mikwamba mia mancha kuchoka mphepete). Nao amagula vincha vilepa vidanchala nchomba. 9Yapo adafika mphepete, adaona mata wa makala pancha ndi pamwamba pake padali ndi nchamba pamonchi ndi mkate.10Yesu wadaakambila, "jina lani baadhi ya nchomba ilo mwavua saino." 11Ndeyapo Simoni Petro wadakwela ndi kuguguza chicha chilepa chidanchala nchomba zazikulu, kiasi cha nchomba 153, japozidali zambili, chincha chilepa sichidang'ambike.12Yesu wadaakambila, "manchani mpate chamasula kukamwa. Palibe ata mmonchi wa apuzila wadaesa kumfuncha, "iwe ndi yani?" Adachiwa kuti wadali mbuye. 13Yesu wadancha, wadatenga uncha mkate, nde wadaninkha, wadachita mchimwecho ndi kwa zincha nchomba. 14Imeneyo idali mala ya katatu kwa Yesu kujilangiza kwa opuzila wake baada ya kuhyuka kuchoka kwa akufa.15Baada ya kumasula kukamwa, Yesu wadamkambila Simoni Petro, "Simoni mwana wa Yohana powa, unikandaine kuliko anyiyawa?" Petro wadanchibu, "etu Ambuye imwe mnchiwa kuti ndi kondani." Yesu wadamkambila, "uwesa mbelele zanga." 16Wadamkambila mala ya kawili, "Simoni mwana wa Yona, Bwa, unikonda?" Petro wadamkambila, etu, Ambuye, imwe munchiwa kuti ndikukondani. Yesu wadamkambila, "Wesa mbelele zanga."17Wadamkambilancho mala ya katatu, "Simoni, mwana wa Yona, Bwa, unikonda?" Naye Petro wadadandaula kwa muncha wadamkambila mala ya katatu, "Bwa iwe unikonda?" Naye wamkambila, "Ambuye, mnchiwa yonche, ndi mnchiwa kuti ndikukondani." Yesu wadamkambila, dyecha mbelele zanga. 18Uzene, uzene, ndikukambila, yapo udali mnyamata udazowelela kuvala nchalu wamwene ndi kupita kwalikonche uko udauna; Nampho yapo siukhale mdala siunyoshe mancha yako, ndi mwina siwakuveke nchalu ndi kukupeleka ukosiuuna kupita.19Yesu wadakamba yameneyo ili kulangiza ndi mtundu uti wakufa ambao Petro wadakamyamikila Mulungu. Baada ya kukamba yameneyo, wadamkambila Petro, "Ndichate."20Petro wadang'anamuka ndi kumwona yuncha opuzila ambayo Yesu wadamkonda wadaachata - Uyu nde uyo wada nchigoneka pa chifua cha Yesu nyengo ya chakudya cha ujulo ndi adamfuncha, "Ambuye, ndi yani siwakuukileni?" 21Petro wadamwona ndeyapo wadamfuncha Yesu, "Ambuye, uyu munthu siwachite chiyani?"22Yesu wadajibu, "ngati nifuna wabaki mpaka yaposindinche, limenelo likuhusu chiyani?" Ndichate. 23Kwa hiyo mau yameneyo yadaenea mkati mwa anyiwancha abalo, kuti opuzila mmeneyo siwafa. Nampho Yesu siwadamkambile Petro kuti, opuzila mmeneyo siwafa, "ngati ndifuna iye wabaki mpaka yaposininche ya kuhusu chiyani?"24Uyunde opuzila wanchocha ushuda wa vinthu hivi, ndi ndaiye walemba vinthu hivi, ndi tujhiwa kuti ushuhuda wake ndi uzene. 25Kuli vinthu vina vambili ivo Yesu wadachita ngati kila limonchi lidakalembedwa, ndiganizila kuti jhiko lonche sidakatosha kuviika kalakala ambavo vidakalembedwa.

Acts

Chapter 1

1Chitabu chija choyamba nidachilemba Theofilo katika mau yonje adaloyayamba nnunu kuchita nikuyaluza. 2Hata siku lija wadatotengedwa kumwamba pajawalipo wadatokwisha kuwagiza kwa mtima mtakatifu waya mitume wajadawachagua. 3Waja wadatothibitisha nafsi yaiye kwa dalili zambili baada yateswa kwake ya kwamba yu wamoyo akiwatumikila muda wa siku arobaijni na kkamba mau yajayausu ufalume wa Mulungu.4Hata pajawadali wadatopezana nao adatowaagiza siwadachoka Payerusalemu bali walindilile ahadi ya baba ambapo mdatovela habari zake kwaine. 5Ya kwamba Yohana wadatobatiza kwa maji bali anyiinu simbatizwe katika Mzimu Woyela baada ya siku zing'ono.''6Basi pajawatopezana wadamfunja wamatokamba, je bwana nyakati hizi ndipo siwabwezele Israeli ufalume? 7Adatowakambila, si njito yanu kujiwa nyakati wala majira baba yajawadayaika katika mamlaka yaiye mwene. 8Lakini simlandile mbavu juu yanu Mzimu Woyela naanyiinu simuwe mashahidi waine katika Yerusalemu na katika Uyahudi wonje na Samaria na hata potela pa nchi.''9Ambuye Yesu yapoadatha kukamba yaya, Adali apenya kumwamba, iye wadanyakulidwa kumwamba. Ndi mitambo idamvinikila kuthi asamuona kwa maso yao. 10Nyengo amapenya kumwamba bwino bwino wamamapita mwazizi, wanthu awili adaima mkatikati mwa anyaio avala nchalu zoela. 11Adakamba, "anyaimwa wanthu Akugalilaya , ndande chiyani mwaima yapa uku ndi mpenya kumwamba?" Yawa Ambuye Yesu apululukila kumwamba siwabwele kwa mtundu umweuja mudamwonela yapo wamapita kumwamba.12Ndeyapo adabwela ku Yerusalemu kuchokela kupili la mizeituni, lili patupi ndi Yerusalemu endedwe la siku lopempha. 13Yapo adafika adapita kumwamba uko amakala nao nde Petro, Yohana, Yakobo, Andrea, Filipo, Tomaso, Batholomayo, Mathayo, Yakobo mwana wa Alfayo, Simon Zelote ndi Yuda mwana wa Yakobo. 14Onche adagwilana ngati munthu mmojhi, pakuti mbila adaendekela ndi mapemphelo. Pamoji ndi anyiayo adalipo wachikhazi, MAriamu amake wa Ambuye Yesu ndi achakulu wake.15Pa nyengo zija Petro wadaima pa katikati panga, ngati wanthu 120, wadakamba. 16Achabale, idali uune, usauna malembo yakwanile, yapo kale mzimu oyela udakamba kupitila mlomo wa Daudi pakati pa Yuda, iye wadaakambila anyiao ada mkana Yesu.17Pakuti iye wadali mmojhi wa ife ndi wadalandila ungo lake la pindu mkati mwa chitandizo.'' 18(Chipano munthu uyu wadakwezedwa pamale kwa pachijha wadalandila pa uomboli wake ndeyapho wadagwa uku wachogoza muthu thupi lidasweka ndi matumbo yake yonche yadali pooneka ndikumwazika. 19Onche amakhala ku Yerusalemu adavela, kwaicho malo yameneyo adapata kwa mkambo "Akeldama" kuti munda wa magazi.'')20mchikalakala cha zaburi mwalembedwa linda malo yake yakale masame ndi pasalolezedwa muthu kukalapo pajna ndiloleza muthu mwina watenge malo yake ya udindo.'21Iyinde yofunika kwaicho mmoji wawachimuna wadachoghozama ndi ife nyengo Ambuye Yesu yapo adachoka ndi kulolwa mkati mwathu 22Chiyambili kutilidwa maji kwa Yohana mbakana siku lija wadatengedwa juu ifunika wakhale mboni wa kuhyuka pamoji kati katindi ife 23Wadaika pachogholo wachimuna awili Yusufu watanidwa Banarba wamatanidwa yusto ndi matia.24Anyaio adapempha ndi kunena imwa Ambuye mujhiwa mitima ya wanthu wonche kwaichi ikani pa danga yuti kati ya awili yawa mwamsankha. 25Kutinga malo ya chitandizo ndi utumiki nyengo Yuda wadachita volakwa ndi kupita pamalo pake. 26Adachita chisanko kwa ndande zao ndi chisanko chidamgwela matia wadawelengedwa pamojhi ndi anyaiwo atumiki kumi ndi mmojhi.

Chapter 2

1Yapo yadafika siku la Pentekosita, wonche adali malo amoji. 2Mwaziziizi kudamuka mau ochokela kumisamba ngati mphep yayikulu nijaza nyumba yonche makhalama wanthu. 3Pamenepo kwayio ngati malilime a moto ziganizidwa zidali pamwamba pawo, aliyembe wake wake. 4Ino adajazidwa ndi mzimu woyela ndi adayamba kukamba mikambo yosayana soyana ngati mmene mzimu adawakambisa.5Nchipano padalepo Ayahudi amene amakhala Muyerusalemu , apempha Mulungu ochokela kila jhiko pansi pa thambo. 6Phokoso yili yapo lidaveka, anthu ambili kolabwela pamoji adali ndi kukayika, chifuko munthu aliyenche adawavela akukamba pa mkambo wakewake. 7Anadabwa ndi kuzizwa, adanena kuti onche yawa sati Agalilea kodi?8Chifuko chiyani ife tiwamvela akukamba aliyenche chimkambo cha kwawo. 9Waparthi ndi Amedi ndi iwo okhala Kumasipotamia Uyahudi ndi Kukapadokia ndi Ponto ndi Asia. 10Ndi Frigia pafulia ndi ku Misili, ndi mbali ya Libia ndi Krene ndi alendo achokela ku Roma. 11Wayahudi ndi na Akrete ndi Walabu yao tikuvela akukamba mumkambo yathu za nchite za phamvu za Mulungu.''12Onse adazizwa ndi kudabwa adakambilana wina ndi mzake, "kodi chimenechi ndi chiyani?" 13Kona ena amasaka ndikuti "yawa akhuta vunyo wa lero."14Koma Petro adakamba pamoj ndi khumi ndi mmjhi, adakkoza mau, adakamba Ayida onu ndi ontche okhala, muno mu Yerusalemu. Velani ndipo muvechetche mau yanga. 15Wanthu yawa salizele ngati mganizia imwe pakuti nthawi ya wana saa tatu umawa.16Koma zidayenela kuchitidwa zokambdwa ndi Yoelmmenel. 17Pazafika masiku othera, Mulungu azakamba ndizathira mzimu wanga kwa wanthu ontche. Wana wanu wamuna ndi akazi azanenela anyamata aezaona vinthu mmasophenya ndi abambo azezalota malota.18Ngakhale pa anchita wanga ndi anchito wa atate wang. Ozakhala masiku amenewo ndizathela mzimu wanga ndi iwo azalalika. 19Ndi za oncha vodibwicha kumwamba ndi vizindikilo pajiko, mwazi moto ndi ulchi toro.20Juwa lizakhala madima ndi mzozi uzakhala mdima, lisadafike siku la likulu la Ambuye. 21Lizakhala kuti aliyenche akayatana pa jino la Ambuye azapulumuka.'22Wanthu a Israeli yomwe, velani mau yaya, Yesu Mnazaleti adali munthu uyu Mulungu adamutuma kwa yomwe. Mulungu adakutchumikizatani vimenevo ndi vaphamvu, vodabwitcha ndi vizindikilo vivo adachita kupitila mwa yiyeyo pakati panu umo mujiwila. 23Kwachifukwa cha maganizo yadalipo kuyambila ndi njelu za Mulungu, adacholchodwa ndi yimwe kwa wnthu owononga, adamphachika ndi kumupha. 24Yomwe Mulungu adamukweza kumuchotcha kuzozoawa za nyifa yake. Chifuko sikundi kutheka kuti iye agwichoe ndi awanthu oipa.25Mmwemo Daudi adakamba za iye nidamuona mbuye nthawi zonse pamaso penga, iye ali kuzonje langa lamanja kuti ndi sinthidwe. 26Chifukwa mtima wanga adili ndi chisangalalo ndi lilime langa udakondwela, ndiso thupi langa langa lizalama ndi chiyembekezo.27Siuzaisiya moyo wanga ku hade, ndi suzolola semuzalole woyela wanu kuti aone choola. 28Mudandiziwisa ine, njala za moyo, uzazichita nizzichwe ndo chisangalalo pamaso panu.'29Amuna yimwe, ndikhoza kukamba choonadi ndi phamvu. chifuko atate wanthu DAvidi, iye adafa adayikidwa m'manda, ndi manda ake alipo mpakana pano pakati pathu. 30Mmene anali mneneli, ndi adaziwa kuti Mulungu adatha kulumbila, kulumbila kwake kuti azaika mmojhi pakati pa mibadwa wake pampando wachifumu. 31Pamene adaona zimenezi mwambanga, ndi adakamba pamwamba kuuka kwa Kristo, ndisadasiyichwe kwa akufa ndi thupi lake silidaole.'32Iye Yesu Mulungu adamuukisa, amene ife taonche ndi mboni. 33Potheza adakwezechwa ndi janja la kwene la Mulungu, nalandila chipangano cha mzimu oyela, kuchokela kwa atate, iye athela pangano imene yemnoe mudaiona ndi kuvela.34Pakuti Davidi sadakwele kumwamba ayi, kama adanena, Ambuye akuti kwa Mbuye wana, khala ku jenje langa la kwene. 35Mbakana pamene ndizaika adani ako chopondapo mapazi yako. 36Mmwemo mnyumba yontcho ya Israeli yozewe kuti uzene Mulungu wanchita iye kukhala Mbuye ndi Kristo. Iye Yesu amene mdanpachika.''37Sopano pamene adamva zimenezi, adalasxidwa mmutima yawo, adamkambila Petro ndi atumwi ena waje abale tichite chiyani? 38Petro adali "lapani ni kubatizidwa aliyenche mjina la Yesu Kristo kupita kukulekeledwa kwa zambi zanu, ndi kupheza mphaso ya Mzimu Woyela. 39Pakuti chipangano alili kwa imwe ndi achiwana wanu ndi kwa ontche ikhala kutari ndi kwawo, ndi ontche Ambuye Mulungu azatana."40Kwa mau amenewa adachita umboni nawadandaulila iwe akamba jipulumusini kum'bacho okholakhola. 41Pamenepo iwo adalandila mau yake adabatizidwa ndipo adaonjezedwa wanthu ngati elfu tatu. 42Ndipo adapitilila kukhala mchipunziso cha alumwi ndi cheyanjano chimoji kumneyo mkate ndi kupemphela.43Koma panabwela mantha pawanthu ontche ndipo vodabwitche ndi vizindiklo vadachidwando wanafunzi. 44Ontche adakhulupilila adali pamoji ndi kukhala ndo vimthu vawo pamoji. 45Ni adagulicha vanthu aneli navo ndi monela yawo na gawila au'mphawi, mmena adafunila.46Mmenemo siku ndi adapitilila ndi maganizo amoji mu hekalu, ndi adatyola mkate ku nyumba zawo ndo adalandila chakudya ndi msangala ndi mtima wona. 47Anamkweza Mulungu ndi kukhala ndi kubali ndi wanthu ontche , Ambuye adaonjezela wanthu sikundi siku amene adapulumuchidwa.

Chapter 3

1Chapano Petro ndi Yohana adali ndiapita paui malopa mapemphelo nthawi yopemphela saa tisa. 2Munthu wakuti wosayenda chibadwile. Wadalindi wabalidwa masiku yonche ndi wadali ndi wagonekedwa pakati pachicheko cha malo yopemphela ya mene yatanidwa mzuri dala kuti wakoze kupempha sadaka kuchokala kwawanthu amapita kunyumba ya mapemphelo. 3Yapo wadaona Petro ndi Yohana awandikila kulowa mnyumba ya mapemphelo wadapempha sadaka.4Petro wadampenyechecha kupunda pamoji ndi Yohana wadamkambila, "tipenye ife." 5Munthu wosayenda wada apenya ndiwa kurupalila kulandila chinthu cha kuti kuchokela kwa anyaiwo. 6Nampho Petro wadakamba, "ndalama ndi chuma ine ndilije nampho chiwene ndilinacho sindikupweche iwe pakati pa jina la Yesu Kristo wa KUnazareti yenda."7Petro wadamtenga pa janja lakela kwene ndi kumkweza kumwamba ntawi kamoji miendo yake ndi vipombono vake va vifupa vake vidapeza mphavu. 8Ndi wammpa kumwamba, munthu osayenda waalowa mapempelela pamoji ndi Petro ndi Yohana ndi walumpa ndi kumuyamika Mulungu.9Wanthu onche adamuone ndiwayenda ndikumkwezeka Mulungu. 10Adajiwa kuti wadali muntu yuja siwamayende wamango kala ndiwapempha sadaka mchicheko cha bwino cha malo ya mapemphelo adajalidwa ndi kuzizwa ndi osazindikil chimene chachitika chifukwa chimene chachokela kwaiye.11Mtundu umo wadali wa agwililila Petro ndi Yohana wanthu wonche kwa umoi wao adatamangila malo yokomenila wa yatanidwa, wa Yerusalemu ndi azizwa kupunda. 12Petro yapo wadaona ichi iye wadaayankha wanthu, anyiimwe wanthu wa Muisraeli chifukwa chiyani muzizwa? Chifukwa chiyani masoyani yapempha viwi kwa ife ngati kuti ife nde tamchita uyu wayende kwa mphavu zatu tawefe kapena maelekedwe yatu?''13Mulungu wa Ibrahimu ndi wa Isaka ndi wa Yakobo, Mulungu waache atate watu amolemekeza mtumiki wake Yesu uyo ndi mmene anyaimwe mnampacho ndi kumkana pamaso pa Pilato. Ingakale iye wadalamula wasiidwe. 14Muda mkano munthu oyela ndi wali ndi ulamulilo pambuyo pake mdafuna munthu wakupa vasiilidwe.15Anyaimwe mdamupa furu wa mtendele mmene Mulngu wadamzusha kuchokela kwa wanthu adafa ife ndi amboni aili. 16Chapano kwa chikhulupi pakati pa jina lake munthu uyu umuona ndikujiwa, wadachitidwa kukala ndimphavu chikhulupi chimene chipitila kwa Yesu yampacha iye mtendele wabwino pachogolo panu anyaimwe mwaonche.17Chapano abale ndijiwa kuti mdachita pakati pausajiwa mwemo umo adachitila achogoleli wanu. 18Nampho vichito vine Mulungu wadakukambilani mwamsanga mwamkamwa mwa olota onche kuti uyu Kristo siwavutike chapano ya kwanila.19Kwaicho lapani ndi mng'anamke dala kuti machimo yanu yakoze kuchochedwa yonche dala kuti zibwele nyengo zo sangalala kuchokela kukalapo kwa atate. 20Ndikuti wakoze kumtuma Kristo mmewa saukulidwa kwa chifukwa,Chanu.21Iyeyo ndimmeneyo chichimichimi jhiko limlandile mpaka nthawi ya kubwezedwela vinthu vonche vimene Mulungu wadavikambila engo za kalekale kwa mkamwa mwa olota oyela. 22Chazene Musa wadakamba Mulungu siwmkweze olota ngati ine kuchokela mwacha abale wanu, simumvenchele chilichonche chimene siwakukambileni anyaimwe. 23Siichokele kuti munthu waliyenhe siwavecha kwa olota mmene siwasowechedwe wochoke pakati pawanthu.'24Yetu, olota oche chichokele Samweli ndi anyiwaa adachatila pambuyo pake odakamba ndi adalalikila nthawi izi. 25Anyaimwe wana wa olota ndi pangizo limene Mulungu wadalichita ndi anya Ambuye ngati ume wadakambila kwa Abraham, "pakati mbeu yako ndi fuko lonche mjiko sizing'anamuka. 26Pambuyo pa Mulungu kumkweza mtumiki wake wadamtuma kwa anyaimwe poyamba dalakuti mpachidwe mwawi anyaimwe kwa kunganamuka pakati pa voipa vanu."

Chapter 4

1Nyengo Petro ndi Yohana yapoadali mkucheza ndi wandhu, anchembhe ndi olonda wa Hekalu ndi Masadukayo adawaendela. 2Adali aipila kupunda kwa ndande Petro ndi Yohana adali mkuwayaluza wandhu kukuza. Yesu ndi kulalika pamwamba pa kuhyuka kwaiye kuchokela kwa akufa. 3Adwagwila ndi kuwaika mgerezampakane umawa ochatila chifuko mokwanila idali mjhulo. 4Nampho wandhu ambili yawodali kuvecha utenga adakulupilila ndi uyinji wa wachimuna yawo adala atokukulupalila, adaganizidwa adali elfu zisano.5Ingakale yapo idafika umawa sikuidachafila, kuti wakuluwakulu wawo, midala ndi ohemba, kwa pamojhi adakamana kuiyerusalemu. 6anasi wamkulu wa nchembe wa dalipo ndi kayafa, udi yoana ndi iskanda, ndi wohehe yawadali ndi achebele wa wamkulu wa nchembe . 7yapoadali awaika petro ndi yohana pakefikati pauo, adafujhe kwa kukoza kutikapena kwa jhina liti mwachite hili?''8Ndipo Petro yapowadahala i wajhala mzimu oyela adkambila, "anyiimwe wakuluwakulu wa wandhu, ndi midala. 9Ngati ife siku yadelo tichimikizidwa kukuza ichitidwe la bwino lidachitidwa kwa mundhu uyu odwala kwa ntundu uti mundhu uyu wadachitidwa umoyo? 10Ebu lijhulikane limenelo kwanu ndi kwa wandhu wonche wa Israeli kuti kwa jhina la Yesu Kristo wa Nazareti, uyo mdamtalamicha uyo Mulungu wadamhyucha kuchokela kchoka kwa akufa, ndi kwa njila yake kuti mundhu uyu waima pano pachogolo panu ndiwakala wa tanzi.11Yesu Kristo ndi mwala uwo anyiiwe omanga mdalipepula nampho ilo lachitidwa kukala mwala wa ukulu wa mphepete. 12Palibe chipulumuchi pa wandhu mwena waliyenche. Kwa mate palibe jhina lena pajhi pa jhiko apachidwa wandhu, iho kwa limenelo tikoza kupulumuchidwa."13Chipano yapoadaona kulimbilika kwa Petro ndi Yohana adajhiwa kuti adali ndi wandhu achimwechi opande njelu, adazizwa adajhiwa kti Petro ndi Yohana adal pamojhi ndi Yesu. 14Kwa ndande adamuona yujha mundhu wadalamichidwa waima pamojhi nawo si adali ndi chindhu cha kunena kupitilila ili.15Nampho yapoadali ato kuwalamula atumi achoke pachogolo pa agulu ndi bwalo, adanena anyiiwo kwa anyiiwo. 16Adanena, sitiachitebwanji wandhu yawa? Ndi zene kuti chidabwecho chodabwicha chachitika kupitila anyiiwo ajhulikana ndi kila mmojhi wakala Kuyerusalemu, sitikoza kulikana limenelo. 17Nampho, kuti chitidwe ili lisidenela mmojhi mwa wandhu ebu sianyindile asadanenancho kwa wandhu waliyenche kwa jhino ili. 18Adatanidwa Petro ndi Yohana mkati ndi kuwalamulila asanena wala kuyaluza kwa jhina la Yesu.19Nampho Petro ndi Yohana wadayankha ndi kwakambila, "ngati ngati ndi uzene pamaso pa Mulungu kukovomelezani anyiimwe kupunda Mulungu, lamulani mwachiawene. 20Chifuko ife sitikoza kusiya kuyanena yochitika yayo tayaona ndi kuyavela."21Pambuyo pa kuwanena kupunda Petro ndi Yohana adasiya ajhipita. Siadakoze kupeza ndande yaliyonche ya kuwalamula kwa ndande wandhu wonche adali kunikoza Mulungu kwa chijha chidali kuchijidwa. 22Mundhu uyowadali kulandila chodabwicha cha kuamichidwa wadapezekova kukala ndi msigu opitilila ndi vyaka arobaini.23Pambuyo pa kwasiya osililidwa, Petro ndi Yohana adajha kwa wandhu wawo ndi kuwaajhinicha yonche yayo wakuluakulu anchembe ndi midela adali kuwakambila. 24Yapoadavela, adakuza mau yawo kwa pamojhi kwa Mulungu ndi kunena, "Ambuye imwe mwa panga kumwamba ndi jhiko ndi nyanja ndi kila chinthu mkati mwake. 25Iwe mmeneyo kwa mzimu oyela kwa pakawa, pa atate watu Daudi mtumiki wa iwe, udanena, ""kwa ndande chiyani wandhu wa ajhiko achita mavulukutyundi wandhu aganizila vichito vosafunike?26Mafumu ajhiko ali pamojhi ndi olamula ali pamojhi pa limojhi ndi wandhu wa mayiko wandhu wa Kuisrali adakomana kwa pamojhi kupitilila atate ndi kupitilila mashili wa iye."27Ndi chichimichimi wonche Herode ndi Pontio Pilato, pamojhi ndi wandhu wa mayiko ndi wandhu wa Israeli, adapezekekana pamojhi pa mujhi umene kupitilila mtumiki wa iwe oyela Yesu, uyoudamtyeka mafuta. 28Adapezekana kwa pamojhi kuchita yonche yayo jhanja lano ndi chikondi chikondi chako chidalamulira kuyambila mmayambo kabla siyadachokele.29Chipano atate, yapenyeni yoofecha yawo, ndi ukawapache watumi waiwe kulinenamau lako posaope wonche kuti. 30Yapoutambaseila jhanja lako kulamicha, chizindikilo ndi vodabwicha vikoze kuchokela kupitila jhina la mtumi wako oyela Yesu. 31Yapo adamaliza kuphembela, malo yayo adasoghana kwa palimojhi lidatingizidwa ndi wonche adajhazidwa ndi mzimu oyela ndi kunena mau la Mulungu popande kuopa.32Gulu lalikulu ya anyiwajha adakulupalila adali ndi mtima umojhi ndi mzimu umojhi ndi palibe ata mmojhi wanyiiwo wadanenakuti chalichonche ichochilimmonja murake chidali cha iye mwene wake. Pambuyo pake adali ndi vindhu vonche paumojhi. 33Kwa mphavu yaikulu atumi adali kulalikila umboni wano kukua kuyhuka kwa atate watu Yesu, ndi kulandila kwa kukulu kudali pamwamba pao wonche.34Padali popande ndi mundhu waliyeche mwanyiiwo wadatedwa ndi vopata, kwa ndande wandhu wonche yao adali ndi chiwembu kumbu cha maliwalakapena nyumba, adavigulicha ndi kupeleka ndalama ya vindhu ivo adavigulicha. 35Ndi kuviika panchi pa myendo ya otumidwa. Ndi kaganidwe kadachitidwa kwa oklupalila, kuchana ndi kila mmojhi ivo wa mavifuna.36Yusufu Mlawi, mundhu kchokela Kukiproadapachidwa jhina la Barnabasi ndi atumiki (imeneyo idatafisilidwa, ndi mwana wa faraja). 37Yapowadali ndi munda adaligulicha ndi kupeleka ndalama, kuziika panchi pa myendo ya otumidwa.

Chapter 5

1Kwa icho munthu mmojhi wamatanidwa Anania ndi Safira mkazake adagulicha munda wao. 2Ndi kubisa ndarama ya kmoi (mkazake wamajiwa) wadapeleka idakale ndi kuiika mmyendo mwa otumidwa.3Nampho Petro wadakamba, "Anania ndande chiyani satana wauchita mtima wakokukamba unami kwa mzimu oyela ndi kubisa chuma cha kumojhi cha munda." 4Nyengo ukali osaguliche, idali osati chuma chako ndi nyapo wagulicha chidali osati panchi pa lamulo lako? Ikala bwanji uganize chinthu ichi mumtima mwako? Siudaanyenge wanthu na wamnyenga Mlungu? 5Povela mau yaya, Anania wadagwa panchi ndi kufa mantha yaajela wanthu onche adavela nkhani iyi. 6Anyamata adaja pachogolo ndi kumveka senda ndi kumpeleka kubwalo ndi kumzika.7Pambuyo pa masaa yatatu, mkazake wadalowa mkati siwajiwa icho chachokela. 8Petro wadamkambila, nikambile ngati mwagulicha munda kwa mtengo huu, wadakamba "yetu ntengo umweo."9Petro wadamkambila, ikala bwanji mavana kumuyesa mzimu wa Ambuye? Penya myendo yao umzika mmunako ili pakomo, sakubale ndi kukupeleka kubwalo. 10Mwachizulumikila wadagwa pamyendo pa Petro ndi kumwalila, anyamata waja adaja mnyumba ndi kumpeza wafa, adam'bala ndi kumpelea ndi kubwalo ndi kumzika pafupi ndi mmunake. 11Mantha yambili yyadaja kanisalonche ndi kwa wanthu onche adavela nkhani iyi.12Vodabwicha vambili vidachokela mkati mwa wanthu kupitila manja ya otumdwa, adali pamoji mu ukumbi wa Suleman. 13Nampho palibe munthu mwina wa payoka walimbikila kuchatana nao, ingakale chimwecho adapachidwa ulemu wa pamwamba ndi wanthu.14Okulupilila ambili adachuluka kwa Ambuye wachimuna ndi wachikazi. 15Kuti adatenga odwala ndi kuaika mmachikandi mmipando kuti Petro yapo siwajipita chitu nchi chake chikale pamwamba pao. 16Pamenepo wanthu ambili adaja kuchokela miji yazungulila Yerusalemu, adapeleka odwala ndi yao ali ndi mizimu yoipa, onche adachilisidwa.17Nampho wamkulu wanchembe wadaima ndi wanthu wadali nao pamojhi (Masadukayo) ;adajalanche. 18Adatambasula, anja ya kuagwila otumidwa ndi kuaika mkati mwa ndande.19Ndi nyengo ya usiku angelo wa Ambuye wadachakula vicheko va ndande ndi kuachogoza kubwalo ndi kukamba. 20Pitani mkaima mu hekalu ndi kuakambila warithu mau yonche ya umoyo uu. 21Yapo adavela chimwechi adalowa mu muhekalu mjengo ya mmalenga kucha ndi kuyaluza nampho wamkulu wa nchambe wadaja ndi onche wagalinao ndikutanicha baraza loche pamoji ndi okota oncha wa lsraeli ndi kuatumakundanda kukaatenda otumidwa.22Nampho atumiki yao adapita saadaapeze kundende adabwala ndi kupeleka mayankho, 23"Tapeza ndande yamangidwa bwino, ndi openyelela aima pakomo, nampho yapo tidachakula sitidaone munthu mkati."24Chapano, nyengo wamkulu wa asrikali ahekalu ndi waakuluakulu anchembe, yapo adavela mau yaya adalowedwa ndi mantha saadajiwe icho chaapeza. 25Munthu mmoji wadaja ndi kuakambila wanthu waja muda aika mndende aima muhekalu atoyaluza.''26Kwa icho wamkulu wa asrikali wadapita pamoja ndi atumiki adajanao nampho saada tenge kwa mphavu ndande amaaopa wanthu, adakabula myala. 27Adaapeleka ndi kuaimika pa baraza ndi kuakambila. 28Tidakukanizani kuyaluza kwa jina la munthu uyu nampho mkali, mwaijaliza Yerusalem mayaluzo yanu ndi kukumbila kutiikila pamwamba patu mwazi wa muthu uyu.''29Nampho Petro ndi otumidwa adayankha tifunika kumlemekeza Mulungu opande wanthu. 30Mlungu wa achiatate watu wadamzyucha yesu mmene nadampa kwa kumuika pamtande. 31Mlungu adamkuzika ndi kumchite wakalejanjala kwene la Mlungu ndi kumchite wamkulu ndi Mpulumusi ndi okuluhula machimo. 32Ife ndi mboni wa vinthu ivi ndi Mzimu Oyera mmene Mlungu wa mchocha kwa yao amlekeza.''33Apungua baraza yupo adavela chimwechi adakwiya ndi kufuna kuapa otumidwa. 34Nampho Farisayo mmoja watanidwa gamalichi mpuzisi wa matauko olemekezeka ndi wanthu onche wadaima ndi kulumula otumidwa ochochedwe kubwalo kwa nthawi yaifupi.35Wadakambila wachimuna a Israel jipenyeleleni ndi chimene mfuna kuachita wanthuyawa. 36Ndande kale lopita theuda wadaima ndikujichita munthu wamkulu wanthu mianne adali kumbuyo kwake wadapedwa ndi yao amani chata onche adasowa . 37Pambuyo pake yuda mgalile mjengo yowlenga wanthu wadaaguza wanthu ambili ndi pambuyo nae wadapedwa ndi gulu loche lidasowa.38Chapano nikukambilani kalani kumphepete ndi wanthu yawa mwaiye achinawene ndande ngati nchito ya wanthu sutaidwe. 39Nampho ngati nchito uji ndi ya Mlungu simkoza kuitimika mkoza kujipeza mpikisana ndi miungu kwa icho adavomelezana ndi mau yake.40Kwa icho adaatana otumidwa mkati ndik atyapa ndi kualamula, asadanenancho mu jina la Yesu ndi kuasiya ajipita. 41Adachoka ndi chimwemwe chifukwa awelengedwa aenela kuvutika ndi osalemekezedwa ndande ya jina la Yesu. 42Kwa icho, kila siku, mkati mwa hekalu ndi kuchokela nyumba mbaka nyumba adaendekela kuyaluza ndi kulalika kuti Yesu ndi Mpulumusi.

Chapter 6

1Chipano pakati pa siku zino nyengo idadi ya opuzila idaongezeka malundu wa Ayahudi wa Kiyunani udayamba pakati Waebrania kwa chifuko ofendwa ndi wachimuna anyaio amayowalika pakati po gawana chakudya kila sku.2Atumiki kumi ndi awili adaudatana msonkhano onche wa opuzila ndi kukamba osati uzene kwatu kulisiya mau la Mulungu ndi kuthandiza pameza. 3Kwa chimwecho bale sankhulani waachimuna saba kuchokela pakati panu wanthu abwino anyiyao ajhalidwa mzimu ndi ulemu yao tikhoza kwapacha matandizo uu. 4Ndi ife tiendekelela nyengo kupempha pakati pa mthandizo wa mau.''5Hotuba yao idaukwadilicha msonkhano onche chimwecho adamsankha Stefano wadajalwa ndi chikhulupi ndi mzimu oyela ndi Filipo Prokoro Nikanori Timoni Parmena ndi nikalao kupulumika kuchokela ku antiokia. 6Akristo wadapeleka wanthu yawa pachogolo pa atumiki yao adapempha ndi pambuyo wadaakila manja yao.7Chimweko mau la mulungu lindaenela ndi idadi ya opuzila idapunda kukuongezeka kumeneko Kuyesrusalemu ndi idadi yaikulu ya makuhani adachivomela.8Ndi Stefano wadajhalidwa ndi mwawi ndi mphavu wamachita vozizwicha ndi langizo lalikulu pakati pa wanthu. 9Nampho pamenepo adakuela wanthu akumojli ochata asinagogi ilo litanidwa sinagogi la Mahuru ndi la Akirene ndi la Waeskanderia ndi wina adali naafunchana ndi Stefano.10Nampho saadakhoze kushindaa ndi ulemu ndi mzimu uwo Stefano wamatumikila pakati pokamba. 11Pothela pake wadaanyenga wanthu wina kwa chisisi kukamba tavela Stefano niwakamba mauya mwano pakati pa musa ndi pakati pa Mulungu.''12Wadaalamula wanthu azee ndi olemba olemba ndi kumpitila Stefano adamgwila ndi kumpeleka pachogolo pa bwalo. 13Wadaapeleka amboni aunami yavadakamba munthu uyu siwasia kukamba mau yaipa pakati pa malo yaya yoela ndi thauko. 14Kwani tamvela niwakamba kti uyu Yesu wa kunazareti siwapawanage pamalo pano ndi kuzing'anamula destuli izozakabizidwa ndi musa. 15Kila mmojhi uyo wadali pakatika bwalo wadayapoleka maso yake kumpemya stefano nao adiaina mphumi yake idali ngati mpumi ya angelo.

Chapter 7

1Kuhani wamkulu wadakamba, "vinthu ivi ni va kweli?" 2Stefano wakamba, "abale ndi anya Ambuye wanga, niveleni ine: Mulungu wa chimwemwe wadamchokela Mbuye watu Abrahamu dyawi yapowali Mesopotamia, kabla siwalame kuharani. 3Adamkambila chokapo, katika jiko lako ndi jama zako ndiupite jiko ilosinikulangize.'4Potela wadachoka jiko la wakala Kuharani, kuchokela pamenepo, baada ya acha Ambuye wake kumwalila, Mulungu adampeleka kujiko ilo, iloakala chipano. 5Siwadampache chalichonche ngati ulithi wake, sipadakale ndi sehemu hata yakuika myendo. Nampho Abrahamu adamuahidi ata kabla siwadapate mwana kuti siwapachidwe jhiko ngati miiki yake ndi ubazi wake.6Mulungu wadanena nae chimwe, yakuti aubazi wake adakakala katika jiko ya ulendo, ndi kuti wenyeji wakuno siachite kukala, atumwa wao ndi kwachita voipa kwa nthawi ya vyaka mia nne. 7Ndi Mulungu wadakamba, silihukumu taifa ambalo silachite mateka, ndi pambuyo pamenepo siachoke ndi kunigwadila katika sehemu ii. 8Ndi adampacha Abrahamu agano la tohara, chimwecho Abraham wadali baba wa Isaka adamtaili sikuya nane. Isaka wadali baba wa Yakobo, ndi Yakobo wadali baba wa mababa zanthu kumi ndi awili.9Mababu zatu adamwonela nchanje Yusufu adamgulicha katika jiko la Kumisri, ndi Mulungu wadali pamoji nae. 10Ndi adamlamicha katika mazunjo yake, ndi kumpacha fadhili ndi ulemu pachogolo pa Farao mflume wa Kumisri. Farao adamchita wakale otawala juu ya Misri ndi juu ya nyumba yake yonche.11Basi kudali udi ujalu udi mazunjo ya yambili katika jiko la Misri ndi Kanaani ndi mababa zatu siadate chakudya. 12Nampho Yakobo yapowadavela kuli vakudya kuori Misri adatuma mababa zatu kwamava yoyamba. 13Katika safali yakawili Yusufu wadajilandiza kwa mabale zake familia ya Yusufu idajulikana kwa Farao.14Yusufu wadauma ambale wake kupita kumkambila yakobo babawao wajekumisri pamoji ndi jamaa zake jumla ya wantu onche nisabiini na tano. 15Chimwecho Yakobo wadachika Kumisri potela wa dafa iye pamoji ndi baba watu. 16Adatengedwa hata Shekemu adazikidwa katika kaburi ambalo Abrahamu wadaligula kwa vipande va ndalama kuchokela kwa wana wa Harani kumene Kushekemu.17Nyengo ya ija ahadi ambapo Mulungu wadamwaidi Abrahamu yapowadasendelela, wanthu adali aongezeka kumene Kumisri. 18Nyengo imeneyo wadaima mfalume mwina pamwamba pa Misri, mfalume uyosiwajiwa kuhusu Yusufu. 19Mmene mflume mwina wadanyenga wanthu watu ndi kwachita voipa baba, ndi kwataya wana wao akanda ili siamoishi.20Katika kipindi chijha Musa wadabadwa, wadali wabwino pachogolo pa Mulungu, wadaleledwa miezi itatu katika nyumba ya baba wake. 21Nyengo wadataidwa binti wa Farao wadamtenga wadamlela ngati mwana wake.22Musa wadayaluzidwa mayaluzo yonche ya Kimisri, idali ndi mphavu katika mau ndi vichito. 23Nampho pamalo pakutimiza vyaka arobaini idamjela katika mmitima mwake kwaendela abale wake, wana Akuisraeli. 24Yapowadamwona Mwisraeli niwachitidwa voipa Musa adamuimila utikulipiza kisasi uyowadali wamamuu amuonela kwa kumbula Mmisri. 25Wamaganizila kuti abale wake siajiwe kuti Mulungu wamlamiecha kwa janja lake nampho siamajiwe.26Siku limachata wadapita kwa baadhi ya Waisraeli anyiyao adali amayambana wadaesa kwagwilichana wadakamba anyabwana anyiimwe ni mabale mbona mlakwilana anyaimwe kula anyaimwe? 27Nampho uyowadamlakwila jirani wake wadamsukumila kwa kutali ndikukamba yani wakuchita mtawala ndi muhumu watu? 28Iwe ufuna kunipa ngati umowampela mmisri julo?''29Musa wadatawa baada yakuvela chimwecho wadali mlendo katka jiko la Midiani ambapo wadali baba wa wana awili. 30Baada ya nyaka arobaini kupita malaika wadamchokela katika jangwa lamapili Sinai katka mwala wa moto mkati mwa matengo.31Nyengo Musa yapowapena moto wadazizwa ndi kustajabu chija wadachiona ndi yapowaesa kuchisendelela ili kuchipenya sauti ya Bwana idamjela idakamba. 32Ine ni Mulungu wa mababa zanu Mulungu wa Abrahamu ndi wa Isaka ndi wa Yakobo. Musa wadatentemela ndi siwadasutu kupenya.33Ambuye adamkambila, "vula vilato pamalo yapo waimani. 34Naona mazunjo ya wantu wanga alipo kumisri navela kudwala kwao nane nachika ili nalamiche ehipano maja nikutume iwekumisri.'35Uyu Musa ambae wadamkana, nyengo yapoadakamba, yani wakuchita kukala mtawala ndi olamua watu? Wadali ndie ambae Mulungu wadamtuma wakale mtawala ndi mkombozi. Mulungu wadamtuma kwa janja la malamulo ambapo wadachokela Musa mtengo. 36Musa wadamchogoza kuchoka Kumisri baada ya kuchitamiujiza ndi alama katika Misri ndikatika nyanja ya Shamu, ndi katika jangwa kwa ntawi ya vyaka arobaini. 37Ni Musa uyu nde uyo wadakambila wantu wa Kuisraeli kuti, Mulungu siwakuinulieni nabii kuchokela pakati pa mabale wanu, nabii ngati ine.'38Uyu ni munthu ambae wadali katika msonkhano jangwani ndi malaika ambae wadanena nae katika phili Sinai, uyu nde munthu ambae wadalandila mau ilolidali la moyo ndi kutipacha ife. 39Uyu ni munthu ambae baba watu adakana kumvechela, adamsukumila kwakutali ndi katika mitima yao adan'anamukila Kumisri. 40Katika kipindi ichimene adamkambila Haruni tikonjele visanamu ivositichogoze, huyu Musa uyoadali wamatichogoza kuchoka kuchoka katika jiko la Misri, sitijiwa ichochidampeza.'41Chimwecho adakonja ndama kwasiku izi ndiadachocha mayamiko kwa chimwecho chosepa ndi adasangalala kwa chifuko cha nchito za manja yao. 42Nampho Mulungu wadang'anamukila ndi kwapacha aabudu utondwa za kumwamba, ngati umoidalembedwa kuchitabu cha manabii, bwa mwanichochela ine mayamiko ya wanyama yaomwachinja kujangwani kwa ntyawi ya vyaka arobaini nyumba ya Israeli?43Mwavomela hema ya kukutania ya maloke ndi ntondwa ya Mulungu refani, ndi picha iyomdaikonja ndi kuabudu wao, ndi sinapeke kwakutali zaidi ya Babeli.'44Baba watu adali ndi hema la kukomanilana la hushuhuda, ngati Mulungu umowadalamulila yapowadakamba ndi Musa, kuti wadaikonja kwa mfano wauja uowauona. 45Ili ni hema ambalo baba watu, kwa nyengo yao adapelekedwa katika jiko ndi Joshua. Ili idachokela chimeue hadi siku za Daudi. 46Ambae wadapata kubali pamaso pa Mulungu, ndi wapempha kufuna makao makuu kwa Mulungu wa Yakobo.47Nampho Seleman wadammangila nyumba ya Mulungu. 48Ata chimwecho wali kumwamba siwakala mnyumba izozamangidwa kkwa manja, ii ngati nabii umowadakambila. 49Kumwamba ni mpango wanga wa ezi, ndi dunia ni sehemu yakuika myendo yanga, nyumba yaiyanji simunimangile? Wakamba Ambuye, Au kuti pamalo panga pomulila? 50Osati janja langa laichita ivinthu vonche?'51Anyiimwe wantu mwene kosi lolimba anyiyao sadatailidwe mmitima ndi mmasikio, kila nyengo mumtimba Roho Oela, mchita ngati baba wanu umoadachita. 52Anyaimwe wantu mwaandila shelia ija yaagizidwa ndi malaika nampho simdaigwile. 53Ni nabii wanji katika manabii ambae baba wanu siadamtese? Adaapa manabii onche adachokela kabla ya ujio wa mmoji ali ni hoki. Ndi chipano muli osati ndi akupa wake pia.''54Potela ajumbe abalaza yapoadavela adapwetekedwa mmitima mwao adamsagila mano Stefano. 55Nampho iye, ikakala wajala roho oela, wadapenya kumwamba kwa makini ndi waduona utukufu wa Mulungu, ndi kumuona Yesu waima janja lakuume la Mulungu. 56Stefano wadakamba,"penya naiona mbingu zavinikilidwa, ndi mwana wa Adamu waima janja la klia la Mulungu."57Nampho wajumbe wa baraza adatimba kelele kwa sauti za amwamba adaziba masikio yao, adamtamangila kwa pamoji, 58adamtaya kubwalo kwa jiko adambula myala, ndi mashahidi adavula nchalu zao kubwalo ndi kuika panchi pafupi ndi myendo yamyamata uyo wamatanidwa Sauli.59Ayapo adali nambula myala Stephano wadaendelea kumtana Ambuye ndi kukamba, "Ambuye Yesu mlandile roho yanga." 60Wadapiga magoti ndi kutana kwa sauti yaikulu, "Ambuye siudawelengela dhambi ii." Yapo wakamba yaya, wadadadula roho.

Chapter 8

1Sauli wadali pamavomelezana ya nyifa yake, siku limenelo nde wadsayamba kwa zunja kinyume cha kanisa lidali Kuyerusalemu. Ni okulupalila onche anyiyao adachoka katika makamu ya Yudea ni Samaria, ila osati ni otumidwa. 2Wanthu akumjiwa Mulungu adamzika Stefano ni kuita maombolezedwe Yakulu juu yake. 3Nampho Sauli wadaliwananga kupunda kanisa. Wadapita nyumba kwa nyumba ni kuwaburuza kubwalo wachikazi ni wachimuna, ni kwa taifa madende.4Okulupalila anyiyao adali achokachoka adali akali kulilakilila mau. 5Filipo wadachika katika muji wa Samaria ni wadamtangaza Mpulumusi kumeneko.6Baada ya wanthu kuvela ni kupenya mambo wachita Filipo, adaika kujipenyelela juu ya chija wadachikamba. 7Kuchoka pamenepo wanthu ambili anyujao adavela, mzim oipa udawachoa wanthu uku alila kwa sauti yaikulu, ni ambili adakosa nkhongono ni asaende adapulumuchidwa. 8Ni kudali ni chisangalalo chachikulu katika muji.9Nampho padali ni munthu mmojhi katika muji uja jnina lake Simoni, uyo wadali wamachita ufiti, ambao wadautumia kwadbwaicha wanthu akamula Samaria, nthawi wamakamba kuti iye ni munthu ofunika. 10Wasamaria onche, tangu wamng'ono hadi wamkulu, adamvechela adakamba, "munthu uyu ni ija nkhongono ya Mulungu ambayo ni yaikulu." 11Adamvechela, chafuko wadazizwicha muda wautali kwa ufili wake.12Nampho, nthawi akulupalila kuti Filipo wadalalikila juu ya ufumu waMulungu ni juu ya jina la Mpulumusi, adabatizidwa, wachimu kwa wachikazi. 13Ni Simoni mwene wadaklupalila. Baada ya kubatizidwa, wadaendekela kukala ni Filipo, yapo wadaona langizo ni vodabicha vimachitika, wadadabwa.14Nthawi otumidwa Akuyerusalemu yapo adavela kuti Samaria yalandila mau la Mlungu, wadatuma Petro ni Yohana. 15Nthawi yapo adaliachika wadapemphela, kuti aulandile mzimu oyela. 16Mpaka muda umeneo, mzimu oyela udali ukali usachikile ata mmoji wao, adali tu abatizidwa uwajina la Ambuye Mpulumusi. 17Ndipo Petro ni Yohana wadaikila manja ni otumikila, wadafune kwapacha ndalama.18Nthawi Simoni yapo wadaona kuti mzimu oyela wachochedwa kupitila kuikidwila manja ni otumikila, wadafuna kwapacha ndalame. 19Wadakamba , "nipacheni ii nkhongono, dala kila uyo sinimulikile manja walandile mzimu oyela."20Nampho Petro wadamkambila nalama yako pamoji ni iwe visowela ktyali, kwa ndande waganiza kuti karama ya Mulungu ipatikane kwa ndalama. 21Lilibe malo katikachinthu ichi, kwa ndande mtima wako siuli wa bwino pamasa pa mlungu. 22Chimweeho basi lapa voipa vako ri kumpempho mlungu pina ulekeleledwe magamizo ya myime walio. 23Chafuko mona uli katika kupachidwa voipa ni kumangidwa chimo.24simoni wadayomkhe nikukamba mpempheni ambuye kwa ndonde yanga pakuti mambo yonohha mwayakamba yakoza kumchokela.25Nthawi Petro ni Yohane yapo adali kupenya ni kulalikila mau la Ambuye adabwela Kuyerusalemu kwa njila imeneyo adalikila mau katika vijiji vambili va Wasamaria.26basi angelo wa ambuye adanena ni filipo ni kukamba mulika ni upite kusini katika njila ipita pomehh Payerusalemu kupita kugaza (njila iyi katika palulu). 27Wadamulikani kupeta pene kudali ni munthu wa Kuethiopia wali ni malamulo yakulu pomehi pakondase maluia wa Kuethiopia waikidwa pamwamba viirithu vake vonche nae wadali wazipita Kuyerusalemu kupempha. 28Wadali mwazifika wakalamgali wasoma chikala cha mlose Isaya.29Chimwechi Filipo wadatamanga liwilo wadamvela niwasoma katika chikalakala cha mlose Isaya wadakamba bwani ujiwa icho uchisoma. 30Muethiopia wadakamba sinikoze bwanji munthu yapo siwaminichogiza wadampempha Filipo wakwele gani ni nukala pamoji naye. 31Mzimu wadakamba ni Filipo, "sendela pafupi ni gari ili ukagwilizane nalo.32Chapamo fungu la malembo ilo wamaliosoma muethu pia ni ii wadachogozedwa ngati mbelele kupita kumachinoni ni kuchinjidwa ningali mbelele wadakala chete wada masule mndomo wake. 33Kwa kusikitichidwa kwake lamulo lake lidachochedwa yani siwakombile obadwane wake? Maisha yake yachochedwa katika jiko.''34Basi buluda wadamfunchha Filipo ni kukamba nikupempempha ni mlose yali uyo wakambidwa ninha ni la Isaya kumtangazila nihani za Mpulumusi . 35Ali mnjila, adafika pali maji, Buluda wadakamba, "penya, pali maji kumtangazila nkhani za Mpulumusi."36Ali mnjila adafika palimaji buluda wadakamba penye pali maji yapa chiani chizwea usisabatizidwa? 37Mau yaya"chimwecho Muethiopia wadayamkha "nikulupalila kati Mpulumusi ni mwona wa Mlungu wadalamula gari liimikidwa. 38Adapila mkati mwa maji pamoji ni Filipo ni buluda Filipo wadambatiza.39Nthawi achoka muja mmaji mzimu wa Ambuye udampeleka Filipo kutali buluda wadamuona wadapita nyile yake washangelia. 40Nampho Filipo wadachokela Kuazoto wadapita katika mkoa uje ni kulaikila mau katika miji yonchhe mpaka yapowadayika Kukaisaria.

Chapter 9

1Nampho Sauli wadaendekela kukamba votisha atavakupedwa kwa opuzila wa Ambuye, wadapita kwa wamkulu wa nchembe. 2Ndi kumphempha barua ndande ya makanisa kumeneko Kudameski, il kuti wakampata munthu uyo wali mkati mwa njila imeneyo, wakale wamuna au wamkazi, wamange ndi kwaapeleka Kuyerusalemu.3Ata yapo wadali pasafari, idachokela kuti yapowadakalibia Kudameski, ghafla idamwakila konche konche dangalila kuchoka kumwamba. 4Nayo wadagwa panji ndi wadavela sauti ndiikamila, "Sauli, Sauli, mbona unitesa ine?"5Sauli wadajibu panji ndi wadavela sauti ndii kambila Sauli mbona unitesa ine? 6Nampho ima lowa kumjini nawe siukambilidwe yayo ifunikana uchite. 7Anjiwaji wanthu adili paulonda pamaji ndi Sauli adakala kacheta ndiavechela Sauli asidaona muthu.8Sauli wadainuka panchi ndi yapowada masula mado yake siwadakoze kuona chinthu adamgwila janja adampeleka mpaka Kudameski. 9Kwa siku litatu siwapena siwakumwa.10Ndo kudali ndi opuzila Kudameski jina lake Anania Ambuye adakamba naye pakatipa kuleso amana ndi wadakamba penya ndilipana mbuye. 11Ambuye adakambila muka ulipakati pa mtaa utari nidwa Nyofu ndi mkati mwa nyumba ya Yuda ndi uka funchile munthu kuchaka Tarso watani dwa Sauli pakuti penya watopempha. 12Ndi wadamwona pakati pa kulesa muthu jina lake Anania ndi walowa ndi kumwiikila maja pamwamba pake ili kuti wapate kupenya.13Nampho Anania wadajibu Ambuye navela habari za munthu uyu kwa wanthu ambili kwa namna yaji umawachitila voipa oyela akumeneka Kuyelusalemu. 14Yapa wali ndi malamulo kuchoka kwa wakulu anchhombe kumgwila kila mmoji uyowalitana jina lako. 15Nampho Ambuye adamkambila mapita pakuti iye ndi chombo cha chagulidwa kwanga walitenge jino langa pachoolo pa pajiko ndi ofumu ndi wana wa Israeli. 16Pakuti sinalangize umo vili vambili ivovidi kutesedwa ndande ya jina langa.''17Anania wa dapita wadalewa muja mnyumba wa damuikila manja wadakamba m'bale Sauli Ambuye Yesu yao adakuchokela pati panjilazapo umoja ani tuma upata kuonancha ndi ujazidwe Mzimu Oyela. 18Ghafla vidagwa pamaso pake vinthu ngati magamba wadapata kuona wadaima wadabatizidwa wadadya chakya ndi wadapata mphavu. 19Wadakala pamoji ndi opuzila kumeneka Kudameski kwa siku za mbili.20Nyenga imeneyo wadamtangaza Yesu mkati mwa makanisa wadakamba kuti iye ndi mwana wa Mulungu. 21Ndi anche davela adashangaa ndi kukamba asati munthu uyu eyawada wawananga anche adali tana jina ili kumeneka Kuyerusalemu ndi yapowadali kwa chifukwa cha kwaamanga ndi kwapeleka kwa wakulu anchembe. 22Nampho sauli wadachitichidwa kutangaza ndi kwa hiti Wayahudi anyiya amakala Kudameski achanganyikawe ndi kusibitisha kuti uyu ndi Kristo.23Baada ya siku lambili Wayahudi adachita maganizo pamaji ili amusipe. 24Nampho mpango wao udajuulikana ndi Sauli adamvizia pakamo usana ndi usiku apte kumuipa. 25Nampho apuzila wake adamtenga usiku adamchicha kupitila muukuta adamchicha panchi mkati mwa chikapu.26Ndi Sauli zapowadafika Yelusalemu wadaesa kujiunga ndi apuzila nampho amata muapa siamakulupalile kutinaye ndi apuzila. 27Nampho Barnaba wadamtenga ndi kmpeleka kwa atumiki ndi adaafo takalela jinsi Sauli umawadamwanila mbuye panjila ndi mbuye umawadakamba ne ndi jinsi Sauli uma wa tandaula kwa ujasili kwa jina la Ambuye Yesu kumeneko Kudameski.28Wadapezana naa yapoadalowa ndi kuchoka Kuyelusalemu wadakamba kwa jina la Ambuya Yesu. 29Ndi wafotokazi ndi Wayahudi Akiyunani nampho adaesa nyenga kwa kumupi. 30Nyinga abale yapoadaji wa chinthu chimencha adamtenga mpaka Kukaisaria ndi ampeleke wapite ku Tarso.31Ndi yapokamisa lonche pakati pa Wayahudi Galilaya ndi Samaria lidali ndi mtendele ndi lidajangadwa ndi kuenda mkati mwa kumwuopa Mbuye ndi ufuru wa Mzimu Oyela kanisa lidakula kaongezaka idadi. 32Ndiyapo idachakokela Petro yapo wamazungukazunguka bendeka zonche za mkaa wadaachikilila waumini aisha mkati mwa maji wa Lida.33Wadamuona kumeneko munthu mmoji jina lake Ainea munthu mmeneya wadati patitanda vyaka nane pakuti wadapeoza. 34Petro wademkambila Ainea Yesu Kristo wakulamiche ukali ndi ujiyalile chitanda chako mala wadauka. 35Ndi wanthu oncha amakala kulinda shareni yapo adamuena munthu uyu adamng'anamukila Mbuye.36Padali ndi opuzila Kuyafa watanidwa Tabitha ila lidatafsilidwa Dorcas uyu wamkazi wadajala nchita yabwina ndi vichito va kulekelela yaye wadachita kwa asauka. 37Idachokela pakati pasiku zimenezo wadadwala ndi wadafa yapoadamsafirisha adamkeza chumba cha pamwamba ndi kumgeneka.38Pakuti lida kalibu ndi Yafa ndi epulila adavela kuti Petro wadali kumeneka adaatuma wanthu awili kwake adampempha uje kwatupi kuchedwa. 39Petro wadauka ndi kuchoka pamoji nao yapoawafika ndampeleka mkati mwa chumba cha pamwamba ndi ofedwa ndadwa ndachamunaa adaima karibu naye ndialila ndi amlangiza koti ndi nchalu izo Dorcas wadasakela nyengo walipamoji nao.40Petro wadaa cha enche kubwala kwa chumba wada gwada magoti wadapempha ndeyapo wadangana mukila ntupi wadakamba Tabitha ukawadamasula maso yake ndi wadamwona Petro wadakala panchi. 41Nde yapo Petro wadamninkha jacha lake wanamwimika ndi yapo wadaafanaokulupalila ndi efedwa ndi achamu nao wadakabidhi kwao wali ndi umoye. 42Chindu ichu chidajulikana kuyafa konche ndi wanthu ambili adamkulupalila mbuye. 43Idachokela Petro wadakala siku zambili Kuyafa pamoja ndi munthu watanidwa simeni akonja vikwetu.

Chapter 10

1Wadalipo munthu mwina wa mmujhi wa Kaisaria jhina lake amamtana Kornelio wadali wa mkulu wa asili kali Waaroma. 2wadali munthu wamaphemphero ndi kukulupalila Mulungu iye ndi amnyumba mwake onche wamachocha ndalama zambili kwa Ayahudi ndi; ndi kumphempha Mulungu masikuli yonche .3Ntawi ya 3:00 usana wadaona vinthu mmaso mphenya angelo Amlungu amjela, angelo wadamkambila Kornelio. 4Kornelio wadamphenya angelo ndi wadali ndi mantha kupunda ndi kunena ichi ndi chiyani mkulu angelo wadamkambila maphemphelo yako ndi mphotilio zako kwa osauka vakwela kumwamba ngati kumbukilo pamaso pa Mulungu. 5Chipano tumiza wanthu kupita ku mujhi wa Yafa akaje ndi munthu mmojhi watanidwa Simoni iyeyo watanidwancho Petro. 6Wakala ndi mkonja vikwetu watanidwa Simoni iye nyumba yake ili mphepete mwa nyanja.''7Pambuyo pa angelo wamakamba naye kuchoka, Kornelio wadaatana anchito wake awili amnyumba mwake,ndi msikali wadali omphembeza Mulungu pakati pa asilikali amamtumikila. 8Kornelio wadaakambila vonche vidamchokela ndi wadaatuma Kuyafa.9siku lidachatila alimnjila nthawi ya 12:00 ndi alipafupi ndi mujhi, Petro wadakwela kudale kukaphempha. 10Ndi wadali ndi njala wamafuna chinthu kati wadye, nampho wanthu yapo amaphika chakudya, wadalangizidwa mmasomphenya. 11Wadaona kumwamba kwa masuka ndichombo chichikha ndi chinthu china ngati nchalu yaikulu idachika panchi pa doti ndi visangwa vake vonche vinai. 12Mkati mwake mudali zinyama za mitundumitundu amiyendo inai ndi zokwawa pa doti ndi visongwa pa doti, ndi mbalame za mulengalenga.13Ndi yadaveka mau kwaiye ''uka Petro iphandi udye, 14nampho Petro wadakamba, osati chimwecho Ambuye ndande sindidadye chinthu chilichonche cho nyansa ndi chasayera. 15nampho mau yadajhancho kaka wili, icho chayelechedwa ndi Mulungu usa chitana chonyansa. 16Ichi chidaoneka katatu, ndichijha chombo chidakwelancho kumwamba.17Petro wali mkati mosokanizika pakati pa yajha wadaona mmasomphenya yatandauza chiyani, ona, wanthu anyiyao adatumidwa ndi Kornelio adaima pachogolo pa chicheko, adafunchila njila yopita kungumba 18Ndi adaona ndi kufuncha ngati Simoni uyo wamatanidwanche Petro wakala paja.19Nthawi imeneyo Petro wamaganiza pakati zija za mmasomphenya Mzimu udakamba naye ona wanthu atatu akafunafuna. 20Ukandi uchike upanchindi ujipita nawo usaopa nawa ndande inendatumidwa. 21Petro wadanchi ndikunena inendeyija mumfunafuna ndande chiya ni mwaja?''22Adakamba mkuu mmojhi jhina lake Komelio ndimuthu olungamandiwakonda mamphmphelo ndi wanthu amkumba bwino jhiko lonche la ayatudi wakambidwa ndimngelo wa mlungu kukutuma kuti upite kunyumba yake kuti wavele utenga kuchokila kwaiwe. 23Petro wadaalandila mnyumba ndikukala pamojhi ndiiye umawa udachatila wadaukandi kupita nawo ndi mabale ochepa kuchokela Kuyafa adachana naye.24siku lidachatila adafika kukaisaria ndi Kornelio wadali walindilila ndi wadaatana pamojhi mabale wake ndimabwenji lake apafupi. Nyengo Peturo wadamuimika ndi kunena ine nane ndimunthu .25Nyengo Peturo walowa mnyumba Kornelio wadamlandila ndi kukwatama makana panchi mmyendo mwake pakumlemeka. 26Nampho Peturo wadamuimika ndikunena ine nane ndi munthu.''27Peturo nyengo ndiwamba naye wadalowa mnyumba ndiwakwama wanthu asonkhanikana pamojhi. 28wadakambila anyamwe mjhiwa kuti osati lamulo la Chiyahudi kugwili zana kupina kuendeledwa ndi munthu uyo osati wa mtundu wanu namho Mulungu wandiza ine sindifunika kumtana munthu waliyencho kuti wonyanya kapina wosayera. 29Nde mate yake ndinda popande mtafu yapo ndidatumidwa chifukwa chaizo kwaichi ndikuncheni ndanda chiyani mdatumidwa ndande yaine.''30Kornelio wadakamba masiku yanai yapita nthawi ngati ino ndimaphemphera nyengo ya 3:00 usana mkati mwanyumba nyengo pachogolo panga ndidaona munthu aima wavala vivolo voyera. 31Wadandikabila Kornelio mphemphelo yako yaveka pamaso pa Mulungu ndi mphoto zako kwa osauka zakala ukilo pamso pa Mulungu. 32kwaicho tumiza munthu Kuyafa wakamtane munthu mmojhi uyo watanidwa Simoni waje kwaiwe uyo watanidwancho Peturo uyo wakala kwa munthu wakonja vikwetu mmojhi wtaamidwa Simoni uyo nyumba yake ili mphepete mwa nyanja. 33Penyelelani milele uwu iye yaposiwajhe siwakambe ndi anyaimwe mulijemo mmalembo aja kale.34Peturo wdamasula pakamwa pake ndi kukamba zenedi ndaona kuti mlungu walinje lusankho. 35Pambuyo pake kila mtundu munthu aliyonche waphemphera Mulungu ndikuchita vichito va bwino wavomeleka kwaiye.36Ujhiwa utenga uo wadauchocha kuchokela kwa wanth Akuisrael yapo wamalengeza nkhani za mtendele kupitila Yesu Kristo uyo wali Mbuye wataonche. 37Mwachinawene wakumjhiwa icho chidachokela Kuyudea yonche ndichidayambila Kugalilaya pambuyo pa ubatizo uwo Yohana wadalengeza. 38Izi zimamkuza Yesu Kristo Mulungu umo wadamtilila mafuta pa Mzimu Oyera ndi kwa mphamvu wadapita kuchita vabwino ndi kulamicha onche amachauchika ndisatuna pakuti mlungu wadali pamojhi ndiiye.39Ife ndi amboni pa vinthu vonche ivowadachita mmaiko ya Uyahudi ndi Kuyerusalemu uyu Yesu uyo adampha ndi kumwamba pa mtanda. 40Uyu munthu wadamucha siku la katatu ndikumchita kujiwikana. 41Osati kwa wanthu onche nampho kwa mambo ni yawo adasakhidwa Mulungu chiyambiepo ife tachinawene timadya naye ndi kumwa naye pambuyo pochidwa kuchokela kwa akufa .42watilamula kulalikila kwa wanthu ndiku tilila umboni uyu ndiye mlungu wadamsankha kukhala olamulika wanyi yaoaliamoyo ndi yao afa. 43Pakati payiye alosi wanche atile umboni kuti uyo wakulupalila waliyonche mkati mwaiye siwakululukidwe machimo kupitila jhina lake.''44Nyengo Petro wamandekela kakamba Mzimu Oyera udaa chikila onche yao amavechela utenga wake. 45Wanthu wajha adagwilana ndi gulu lokulupalila aumbalidwa onche adaja ndi Petro adadabwa chifukwa cha mphaso ya Mzimu Oyera uyo wadamwazidwa kwa wanthu amaika oyera uyo wadamwazidwa kwa wanthu amaiko.46Pakuti adavela anyiyawao amaiko akamba mikambo injake ndi kumphemphela Mulungu Petro wadayankha. 47Walipo munthu waliyenche wakoza kucheleza mmojhi kuti wanthu oyera ngati ife. 48Ndeyapo wadaiamula kuti abatizidwe mjhina la Yesu Kristo pambuyo adampempha wakale nao masiku yakuti.

Chapter 11

1Akumwa ndi abale waja adali ka Yuda adaniva kati ametundu adalandila maua ni Mulungu. 2Pamene Petro adabwela Kuyelusalemu gulula wanthu ochelidw aadakangana nayo adakamba uti, 3''Wemvina ndi wanthu asadulidwa ndi kudya nazeo pamoji.''4Nampho Petro adayamba kukamba vimene vedamchikitila kwa aliyentche. 5Nidali kupemphera kamji wa yopa ndedaona masomphenya chotengela chikusika kuchokela kumwamba ngati chisalu chongilandwa nichonga zake zinayichidatichika pedali ine. 6Nidachipenyetchake ndi kuchiganizila nedepenya nyama za mayendo inayi ni vilombo va pajiko la pentche ni vokwawa ni mbolame amlengalenga.7Nevala mau okamba ndi ime akuti Petro ukayepha ni udye. 8Koma nidati iyayi Ambuye sunenadije kanthu kalikonche koepa kapena kosakanjeka sekadelewa mtanizo mwanga nikale lomwe. 9Koma mau anabwelantche kuchokela kumwamba yicho Mulungu wa chiyeletcha usachetae chakada. 10Yachi chidachitichwa katatu pambuyo pake chidatengechwa kupite kumwimba11Tapenyani nthawi yomwe wanthu ustahi adaima pabwalo pa nyumba iyo tedalimo adatumuedwa kukaiseke kubwela kwa ine. 12Ngumu udanikwambela kuti nepite nawo osalekanit cha nwo ndi wenthu sita adanipelekaga uleplapitaka nyumba ya munthu wine. 13Adatikambila umo udamuonela malaika adayemila mteti ni wa nyumba nikakamba lumani wanthu kuyopa akamutenga Simoni otanidwa Petro. 14Agakemba ujumbe kwa mwe umene ugaombela ni abali wako ontche.''15Pamene nidayamba kukamba nawo Mzimu Oyela anabwela pamwamba pawo ngati mene adabwela pa ife poyamba paja. 16Nikubuka maze Ambuye adakamba Yohane adawabatiza ndi maji, koma yizafika nthawa yomene muzabatizadwa ndo Mzimu Oyela.''17Ndithu ngati Mulungu wachotcha zawadi ngati adetipatche ife panene tidakhupilila Ambuye Yesu kristo ine ndani kuti kumpinga Mulungu? 18Pamene adavela zimenezi adakhala Mulungu ndikukamba Mulungu wapeleka kulapa ngakhala kwa anutunefu.''19Basi okhulupilila mazunjo yadayamba pamene Stefano adaphedwa ndifo adasalana kwinakwa na Kuyelusalemu akhulupilila adapila kutari kufomuke kipolo mpakana ku Antiokia. Adakamba uthenga ohusu Yesu Kristo yekha basi kwa Ayuda osati kwa aliyentche. 20Koma mbali ya wina ni wanthu ochokela ku Kipro ndi Krene, adabwela Antiokia ndi kukamba Wayunani ndi kukalika za Ambuye Yesu. 21Nizanja la Ambuye lidali pamoji ndi tuu, ndi zanthu ambili adakhulupilila ndi ang'anamuka Ambuye.22Ndi nkhani zao zidafika mmakutu mwa kanisa lonche la Kuyerusalemu, ndi adamtuma Barnaba apite mpakana ku Antiokia. 23Yapo adafika nikuona mphanile Mulungu adakondwa kwambili, adakulimbikitcha onche kukhala ndi Ambuye m'mtima wawo. 24Chifuwa adali munthu wabwino ndi adajazidwa ndi Mzimu Oyela ndi chikhulupilil ni anthu ambili adaonjezeka kwa Ambuye.25Pambuyo Barnaba adapita Kutariso kukamuona Sauli. 26Yapo adamupheza, adabwelanayo Antiokia. Yidali chaka chatunthu, adabwela pamoji ndi kanisa lidephungasa wanthu ambili. Ndi ophunzila adatanidwa Akristo koyamba ku Antiokia.27Ni panthawi yameneyo wanafunzi kapena olosa ambili adabwela ku Yerusalemu mpakana ku Antiokia. 28Mmoji wao ndi Agabo nde jina lake, wada adafina nde mphamitu ya Mzimu Woyela adalosa kuti pazakhela njala yejikulu pajiko lontche lapasi njaleyo yidabweladi pa nyongo yake ya Klaudio.29Pamenepo Akristo aja akhulupilila kutumuza thandizo kwa abale okhala ku Yudea, kuti aleyontche atumize molingana ndi kupata kwake. 30Zimenezi zidachitikadi, adatuma Banabasi ndi Saulo, kukapelika thandizolo kwa akulu amphingo.

Chapter 12

1Ntawi, imeneyo fulo Helode wadalangiza jauja lake kwa ochepa nche ome anchokela mkati thagulu dala apeze mavuto. 2Wadamopa Yakobo mbalewake Yohana kwa chikwanje.3Pambuyo pakupeuya kuti iwakadwila Wayahudi wadamgwila ndi Petro loncho liidali ntawi ya mikate yo chuchuluka. 4Yapo adamgwira adamwika mndende ndi adaika maguru yanai askari dalakuti kumpenyelela wama kurupalila kumpeleka kwawantu pambuyo pa Pasaka.5petro wadailadwa mdende nampo mapeupelo yadachifidwa kwa mpavu ndigulo ndande yaiye kwa mrungu. 6Siku wakarli herode osapifa kumcho cha usiku omweo Petro wadali wan'gona pakatikafi pa azankongo awili ukuwamangidwa ndi vingwe viwili ndialonde alipa chogoro pachicheko ukundi ndi alipenyelela ndende.7Peuyawi malaika wa Mulungu mwazizili wadachokela ndi dangalila mkati wada mwenya Petro mmbalati ndi kumuucha ndiwakamba, ''uka msanga nde pamenepo vingwe wadamangidwila vida masuka kuchokela mmanja mwake." 8Angelo wadamnenela ''valancharo zako ndivilato vako'' Petro wadechifa chimwencho angelo wademkambila vala chovala chako undichate.''9Mmwemo Petro wada mchata angelo ndiko choka kubwalo, siwada ziudikile chimeve chifa chitidwa ndiangelo ngati chazene wamaganize waona ndoto. 10Pambuyo pakupyeuka pa ulinda oyamba ndipaka wili atafika pachicheko cha chichuro cholowela kupita mkati mwamuji chidamasuka chene chifuko chao adachoka kubwalo adachika mopifa kenake angelo wadamsia.11Petro yapo wadafifiwa wadakamba'' chapamo nda vawanazo kutimulungo wadamtuma angelo wake dala kundi chocha nikati mwa mauja ya Herode ndikwazofunikila za wantu woche wa Kuuyahudi.'' 12Pambuyo poyajiwa yaya wadaja mnyumba ja Mariam majiwake Yohana mmene wali Marko wantu a Mulungu ambili adakalila limoji ndiapempela.13Pamene wadawodika pachicheko choka rizidwa mtumiki mmoji wamkazi wa damidwa lode wadaja kummasula. 14Yapo wadejiwa kuti mau ya Petro kwa chisangalalo wadepela kumasula chicheko pambuyo pake wadatawila mkati mwachipinda, ndi kwa ajiwiche kuti Petro waime pachogoro pa chicheko. 15Mmwemo adakamba kwaiye, "iwe ndi ubwabwazika" napo wadalangiza maso kuti iyedi adakamba, "mmeneyo ni angelo wake."16Nampho Petro wadaendekela kumasura chicheko yapo adamasula chicheko adamuona ndi adazizwa kupunda Petro wadaakambila akale kachete mwa janja. kachete kachete ndi wadaakambila mmene Mulungu wamchochela mudende wakamba, 17"Akambileni nkani izi Yakobo ndi abale wake, "pambuyo wadachoka ndi kupita malo yena.18Yapo idari usana kudali ndi madandaulo kupunda pakati pa alonda kuchokela chimene chachokela kwa Petro. 19Pambuyo pa Herode yapo wadamfuna ndi oamuona wadaafuncha alonda ndi kuchocha lamulo kuti apedwe wadapita kuchokela ku Uyahudi mpaka ku Kaisaria ndi kukala kumeneko.20Herode wadali ndimpwai pamwama pa wanthu atilo ndi Sidoni adapita kwa umoji wao kwaiye adakala ndi ubwenji ndi brasto otandaza wake wamkuru wajiko dala kuti waatadize potela pake adapempa mtendele chifukwa jiko lao lidalandila chakudya kuchokela jiko la wamkuru wa jiko. 21Siku lidaganizilidwa Herode wadavala nchalu za ulamulilo ndi kukala pampando wake wa mkuru wa jiko ndi kwaakambila.22Wanthu adamenya mapokoso, "Yaya ndi mau ya Mulungu osati ya wantu!" 23Mwa zizizi angelowadammenya, chifukwa siwadampache Mulungu ufuru wadajedwa ndi mkango ndi wadamwalila24Nampo mau la Mulungu lidakula ndi kumwazika. 25Pambuyo pa Barnaba ndi Sauli kumalizila chitandizo chao adachoka pamenepo kubwelela ku Yerusalemu adamtenga Yohana mmene jina lake la kubadwa ni Marko.

Chapter 13

1Chipano pa kanisa la Antiokia padali ndi wena wa olosa ndi oyaluza adali Barnaba Simeoni (wamatanidwa Nigeri) Lukio wa Kukirene (mbale wake osati wa mwazi wa Herode mchongozi wa mkoa) ndi Sauli. 2Yaupa adali kulambila atate ndi kumanga mzimu oyela wadanena nipatulileni pambhepete Barnaba ndi Sauli, aichite njhito vyo natanila. 3Pambuyo pa kanisa kumenja, kupembha ndi kuike manja yowo kumwa kwa wandhu yawa akasiya apite.4Kwa icho Barnaba ndi Sauli wadamlemekeza Mzimu Oyela ndi kuchika kupitila kuseleukia; kuchoka kumeneko adapitila mnyanja ya mchele kupitila kuchilumba cha Kipro. 5Yapoadali pa mujhi wa Salami adalalikila mau la Mulungu pa masinagogi ya Wayahudi mmwemoncho adali pamojhi ndi Yohana Marko ngati otangatila wawo.6Yapoadapita pa chilumka chonche mpakana kupafo adapeza mundhu nnajhi mfiti Myahudi ohosa wa unami mmene jhina lake lidali Bar Yesu. 7Mfiti uyu wadagwili zana ndi liwali Sergio Paulus uyowadeli mundhu wa njelu. Mundhu mmeneyo adalalika Barnaba ndi Sauli kwa ndanda adafuna kuvela mau la Mulungu. 8Nampho elima '' yujha mriti'' (mmwemo ndimo jhina lake limado ngosoledwa) adawachucha; adayesa kumnganamula yujhe liwali achoke kuchikulupi.9Nampho Sauli uyowadatanidwa Paulo wadali wajhazidwa ndi Mzimu Oyela wadamcimikizila maso. 10Nde anane ''iwe mwana wa chilombo wajhazidwa ndi mitundu yonche ya kunyenga ndi kwonda. iwe ni mdani wa kila ntundu wa malinga siusiya kuzinganamula njila za atate izo zaongoka bwanji siukoze?11Chipano penyani jhanja la tate lilipo pamwamba pako ndi siukale osapenya siuliona gehua lava nyengo ''mara kamojhi'' punduulu ndi mdima vidangwa pamwamba pa Elimas wadayamba kuzungulila pajha ndi wapembha wandhu amchogoze ka kumgwila jhanja. 12Pambuyo pa liulali kupenya ichochachokela wakulupilila kwa ndande wadazizwachidwa kwa mayaluzo kukuza atate.13Chipano paulo ndi mabwenji wake adayende ulendo mmanji kuchokela kupafo ndi kufika kuperge pa pamfilia nampho Yohana adawasiya ndi kubwela kuyerusalemu. 14Paulo ndi bwenji lake adayende ulendo kuchokela kuperge ndi kufika ku Antiokia ya pisidia kumeneko adapita pa sinagogi siku ya sabata ndi kukala panjhi. 15Pambuyo pa kusoma malamulo ndi olosa achogoleli wa sinagogi adawatumazila utenga kunena Abale ngati mulinao utenga wa kutila mtima wandhu pano nenani.''16Kwa icho Paulo wadaima ndi kupila Jhanja kunena wachimuna aku Israel ndi anyiimure irewe mvumeleza mlungu vechelani. 17Mulungu wa anyiwaja wandhu wa Kuisraeli adewasagula anyatate wanu ndi kuchita wandhu ambili yapoadakala pa jhiko Kumisri, ndi kwa jhanja lake kukwezedwa adawachogolela kubwalo kwake. 18Vyaka arobaini adadikilila pa pululu.19Pambuyo pa kuyawananga mayiko saba pa jhiko la Kukanaani adapacha waudhu watu jhiko lawo kwa kupachidwila. 20Vochokela ivi vonche vidachokela kupunda pa vyaka mia nne ndi hamsini pambuyo pa vinthu ivi vonche Mulungu adawapacha olamula mpakana Samwel mlosi.21Pambuyo pa yaya wandhu adapembha mfumu mwemo Mulungu adapacha Sauli mwana wa Kishi mundhu wa kamu la Benjamini kukela ufumu kwa vyaka arobaini. 22Ndipo pambuyo pa Mulungu kumchocha pa ufumu adamkweza Daudi mwana wa Yese kukala mfumu wawo idali ndi kukaza Daudi kufi Mulungu wadanena nampeza Daudi mwana wa Yese vukala mundu okondechedwa ndi mtima wangai uyo wasichite kila kandhu nichikondo.'23Kuchoka ku ukoo wa mundhu uyu Mulungu waipelekela Israel Mpulumuchi Yesu ngati umowadapanganila kuchita. 24Limenelo lidayamba kuchokela mmbuyo mwa Yesu kujha Yohana payamba wadalalikila ubatizi wa kelapa volakwa kwa wandhu wonche wa kuIsrael. 25Nayencho Yohana yapo wadali kumalizila njhito yake wadanenae mganizila Ine ndi yani? Ine osafi yujha nampho vechelani wakujha kumbayo kwanga sinifunika kumasula sabato za myendo yake.'26Abale wana wa kamu la Abrahamu ndi wajha yawo pakati panu mmulezi mekaza Mulungu ndi kwa chifuko chatu kuti kutenga uwe wa Chipulumuchi watumidwa. 27Kwa anyiiwo akala Kuyerusalemu ndi wakwalamula wao siwadamzindikile kwa umo wali ndi poje siada uzindikile utenga wa olosa uwo usomedwa pa sabato; kwa icho adakwanilicha utenga wa olosa kwa kumlamula nyifa Yesu.28Ingikale siwadapate ndande ya bwino kwanyifa mkati mwake adampembha Pilato amphe. 29Yapo adamaliza vocheta vomche vidalembedwa kukuza iye adamchicha kuchoka pamtego ndi kuungoneka mmanda.30Nampho Mulungu wadamhyucha kuchokela kwa akufa. 31Wadaonekana kwa masiku ya mbili kwa anyiwajha adapita pamojhi ndiye kuchokela ku Galilaya kupitila Kuyerusalemu. Wandhu yawa chipano ndi amboni.32Mmwemo tikupelekelelani nkhani za owino kukuza vipangano adapachidwa achambuyatu. 33Mulungu adaika vipangano ivi kwaife, wana wawo, pa limenelo adamhyusha Yesu ndi kumbwezancho pa umoyo. Ili nalo lidale mbendedwa pa Zaburi ya kawili; iwe ndi mwana wanga, lelo nakala atate wako. 34Namponcho kukuza uzene ndi kuti adamhyucha kuchoka pa akufa kuti tuphi lake lisadawanangika, okamba chimwechi; "sinikupache kuyela ndi mwawi wazene wa Daudi'35Iyi ndiyo ndande kunena nancho p Zaburi yena, "siulamula oyela waiwe kuchiona choola.' 36Pakuti pambuyo pa Daudi kutumikila chikondi cha Mulungu pa chibadwa chake, wadagona, wadagonekezedwa pamojhi ndi anyatate wake, ndi kuwena kuwanangika, 37Nampho uyowahyushidwa ndi Mulungu siwadaone kuwanangika.38Mmwemo ndi ijhiweke kwa anyiimwe,abale, kupitila mundhu uyu, chilekelelo cha machimo. 39Kwa iye wakulupalila wawelengeda malinga ndi vichito vonche ivo matauko ya Musa sidayakapatila malinga.40Mmwemo basi kalani ojhipenyelela kuti chindhu adachikambilila olosa sichidachokela kwa anyiimwe. 41Penyani, anyiimwe mpepula, ndi kuzidwa mkawanangikidwe, kwa kuti mchita nchito masiku yanu, nchito iyo sinikoze, kuikulupalila atangati muudhu siwakufotokaozeni. Nyengo paulo ndi barnabe yapo adachoka wandhu adapenthe ake mbe mau yaya siku ya sabato ikujha.''42Nyengo Paulo ndi Barnaba yapo adachoka, wandhu adapembhe akembe mau yaya siku ya sabato ikujha. 43Nyengo nsoghano wa sinagogi yapoodata wajahudi ambili ndi opulumuka omiliha adawachata paulo ndi barrabe yawo atkambe nawo ndi kwa suimikuza aendekele pa neema ya mulungu.44Sabato iyoidachatila pafupi pa mujihi wa mphuphu udasoghano kuvechela mau la Mulungu. 45Wayahudi yapoadaona msonghano adajazidwa ndi nchanje kuyenena mau yadachucha viudhu vidakambidwa ndi Paulo ndi kumtukwana.46Nampo Paulo ndi Barnaba adanena kwa mphamvu ndi kunena idali ndi ya kukulupalila kuti mau la Mulungu likambililidwe pakuyamba kwa anyiimwe pauti mulitaila kwa kutali kuchoka kwa anyiimwe ndi kujhiona kuti simafunikile umoyo opitilila penyani siti wang'anamukile ajhiko. 47Ngati umo Atate atilamulila kunena nakuikani anyiimwe ngati dangalila kwa wandhu ajhiko kuti mpeleke chipulumuchi kwa madela yonche ya jhiko.''48Mayiko yapo adavela ili adakondwa ndi kulemekeza maula atate ambili adasagulidwa kwa umoyo opitilila adakulupalile. 49Mau la Atate lidainela jhiko lonche.50Nampho wayahudi adapempha yawoadajhichocha ndi wachikazi chamuhimu naponcho ndi ochogoza wa muijhi yaya yadasongozela mavuto kwa Paulo ndi Barnaba ndi kwataya kubwalo pa malile ya mujhi. 51Nampho Paulo ndi Barnaba adakung'undha malifumbi ya myendo yawo pakutela adapita ku mujhi wa Ikonia. 52Ndi opinzila adajhazidwa ndi chimwemwe pamojhi ndi mzimu oyela.

Chapter 14

1Idachokela Kuikonio kuti Paulo ndi Barnaba adalowa pamoji mu sinagogi la Ayuda ndi kucheza mtundu umene gulu lalikulu la wanthu Ayuda ndi Ayunani adakulupilila. 2Nampho Ayuda alije ulemu adasongozela njelu wanthu samanjiwe Mulungu ndi kuachita akale ipa kwa abale.3Kwa icho adakala kumene nyengo yaitali ndi acheza kwa mphavu ya Mulungu wamachita zokuza utenga wa chimwemwe chake wadachita chimwechi vodabwicha vichitike kwa manja ya Paulo ndi Barnaba. 4Nampho malo yayakulu ya muji yadagawika wanthu akumoji adali pamoji ndi Ayuda ndia kumoji adali pamoji ndi otumidwa.5Nyengo osajiwa Mulungu ndi Ayuda amayesa kuakambila achogoleli wao kuachitila voipa ndi kuaponya myala Paulo ndi Barnaba. 6Adajiwa limenelo ndi kutawila mu miji ya likaomia Listra ndi Derbe ndi malo yazungulila paja, 7Ndi kumeneko adalika utenga.8Ndi Kulistra kudali munthu mmoji wadakala walije mphavu mmyendo mwake olumala chiyambile mmimba mwa amake siwadaendepo. 9Munthuyu wadamvela Paulo ndi wakamba Paulo wadampnya molimbikila ndi kuona kutiwadali ndi chikulupi cho chilichidwa. 10Kwa icho wadamkambila kwa mphavu imakwa myendo yako yuja munthu wadadumpha kumwamba ndi kuyamba kuenda.11Gulu yapo lidaona icho wachila Paulo adakazomoka mu mkambo wa kilikanio milingu yatichikila mu mtundu wa wanthu. 12Adamtana Barnaba ''Zeu'' ndi Paulo ''Herme'' ndande wadali okamba wamkulu. 13Wamkulu wa nchembe wa Zeu iye hekalu lake lidali kubwalo kwa muji wadapeleka mphango wa ng'ombe ndi mtungo wa madua mbaka pakomo pa muji iye ndi gulu la wanthu adafuna kuchocha nchembe.14Nampho otumidwa Barnaba ndi Paolo yapo adavela yaya adapwatula vovala vao ndi mwamsanga adapita kabwalo pagulu ndi adalila. 15Ndi kukamba anyiimwe wanthu ndande chiyani muchita vinthu wi? Ife nafe wanthu tili ndi magani zo ngati yanu tikupelekelani utenga wabwino kutimng'amuke kuchoka kuvinthu vopande mate ndikumchota Mlungu walimoyo wadalenga kumwamba ndi fiko la ponchi ndi myanja ndi vilimkatimwake. 16Nyengo yopita wadaavomeleza wanthu osachata Mlungu kuenda mnjila zao.17Nampho ikali siwadachoke popande mboni mmenemo wadachita bwino ndi wadaapacha mvula kuchoka kumwamba ndi nyenga yobalicha waapacha chakudya ndi chimwemwe mmitima mwao. 18Pa mau yaya paolo ndi Barnaba kwa mavuto adaakaniza gulu kuachochela nchembe.19Nampho akumoji mwa Ayuda kuchoka Kuantiokia ndi Kuikonio adaja kukambila gulu adambula myala paoloo ndi kumkwekweta mbaka kubwalo kwa muji ndi amaganiza wafa. 20Ingakale chimwecho opunzile adali pafupi ndi iye alimalima wadauka adalowa mmuji siku ya kawili wadapita kudebe ndi Barnaba.21Yapo adapoyaluza utenga wa Mulungu mmoji uja ndi kuachita opunzila ambili, adabwela Kulistra mbaka Kuikoniamu ndi mbaka Kuantiokia. 22Adaendekela kulimbikila mizimu ya opunzila ndi mtima kuendekela muchikulupi, "wadakamba nditu tilowe mu ufumu wa Mulungu kupitila mavuto yambili."23Yapo adasankha waakulu akansa la okulpilila ndi atokuapemphela ndi kumanga osadya, adaaika mmanja mwa Ambuye iye anyiiwo amamkulupilila. 24Ndipo adapia mu Pisidia, adafika ku Pamfilia, 25Nyengo amacheza mau mu Perga, adachika kupita ku Atalia. 26Kuchokela kumene adakwela sitima mbaka Kuantiokia kumene adali ajichocha, kwa lisungu la Mulungu kwa ndande ya nchito imene chapano adali aikwanilicha.27Yapo adafika Kuantiokia na Kuakusa wanthu pamojhi, nde adachocha nkhani ya vinthu vimene Mulungu waachitika ndi ntundu wadaachakulila chicheko cha chikulupi kwa wanthu a Maiko ina. 28Adakala kwa nthawi ya itali ndi opunzila.

Chapter 15

1Wanthu akuti adachika kuchokela Kuuyahudi ndi kuwayaluza achaabale adakamba ''ngati simuumbalidwa ngati dongosolo la Musa simukhoza kuomboledwa''. 2Nyengo Paulo ndi Barnaba yapoadali ndi mpikisano ndi kukambilana pamojhi nao acha abale adalamule kuti Paulo Barnaba ndi wia apite Kuyelusalem kwa atumiki ndi okota kwa chifuko cha funcho ili.3Kwa chimwecho pakutumidwa kwao ndi kanisa adapitila Kufoinike ndi kusamaria kulengeza kunganamulindua maganizo. Adapeleka chisangalalo chachikulu kwa achaabale onche. 4Yapo adajha Kuyerusalem adakhalbishidwa ndi kanisa ndi atumiki ndi azee ndi adazifikicha nkhani za vinthu vonche ivo Mulungu wavichita pamojhi nao.5Nampho wanthuakuti yao adavomela yaoadali pagulu la afalisyo adaima nd kukamba nimate kuwaumbala ndi kuwalamula aliguile thauko lamusa. 6Chimwecho atumiki ndi azee adaima pamojhi kuiganizila ii nkhani.7Pamalo pakamba nyengo ya itali, Petro wadaima ndi kukamba kwa anyaiwo, "abale mujhiwa kuti nyengo ya bwino iyoyapita Mulungu wadachita lisankho pakati panu, kuti kwa mlomo wanga maiko yavele mau la ulaliki, ndi kuvomela." 8Mulungu, uyo waijhiwa mitima, watilila umboni wa apacha mzimnu oela, ngati umo wadachitilakwathu. 9Ndi siwadakonje kusiyana pakati pathu ndi anyaiwo, wadaichita mitima yao bwino.10Kwa chimwecho kwa chiyani mumuesela Mulungu kuti mwike nchinda pamwamba pa makosi ya opuzila yayo ata acha atate wanu ata ife sitikhoza kuembekeza? 11Nampho tivomela kuti sitilamichidwe kwa mwawi wa Ambuye Yesu, ngati umo adali.''12Msonkhano onche udakhala chete yapoamamvechela Barnaba ndi Paulo yapo amaichocha nkhani ya langizo ndi vozizwicha ivo Mulungu wadavichita pamojhi ndi anyaiwo pakati npa wanthu amaiko.13Yapo adasiya kukamba yakobo wadayankha ndi kukamba abele nivecheleni. 14Simoni wakambilila payamba mulungu kwa mwawi wadaathangatila maiko kuti wajhipatile kuchoka kwao wanthu kwa chifuko cha jhina lake.15Mau ya olosa yadavomelezana ndi ili ngati umo lidalembedwela. 16Pamulo pa vinthu ivi sinibwele ndi kuimangancho hema ya Daudi iyoidagwa panchi sindiikweze ndi kuibweezela uzene wake. 17Kuti wanthu anyiyao akhalila amfunufune ambuye pamojhi ndi wanthu amaiko yao atanidwa kwa jhinalanga. 18Umu ndeumo wakambila ambuye uyo wachita vinthu ivi vijhiwikana kuyambila nyengo za kale.19Chimwecho basi ganizo alanga ni kuti sitidaapacha vuto wanthu amaiko amng'anamukila mulungu. 20Nampho tilembe kwao kuti ajhipatule patali ndi kuwanangika kwa chifani kumbilo la uhule ndi ivovamangidwa ndi mwazi. 21Kuchokela abanzi wa okota kuli wanthu pakati pa kila mujhi olalikila ndi kumsoma Musa pakati pa masinagogi kila sabato.''22Kwachimwecho idaonekana kuti idaakwadilicha atumiki ndi okota pamojhi ndi kanisa lonche kumsankhula Yuda uyuwadatanidwa Barsaba ndi silas adali ochogaza kanisa ndi kwaatuma kuantiokia pamojhi ndi Paulo Barnaba. 23Alemba chimwe atumiki okota ndi abale kwa abale amaiko anyiyaodali kuantiokia kushamu ndi kukilikia salamu.24Tidavela kuti wanthu akuti yaositidaapache lamulo limenelo adachoka kwathu ndi wadavuticha kwa mayaluza yapeleka vuto mmitima mwanu. 25Kwaicho yaonekana bwino kwathu taonche kusankula wanthu akwatuma kwanu pamojhi ndi okondedwa wanthu Barnaba ndi Paulo. 26Wanthu yao adakhaikicha umoyowao kwa chifuko cha jhina la Ambuye Yesu Kristo.27Kwa chimwecho tamtuma yuda ndi sila saakukambileni vinthu vimenevo vonche. 28Pakati yaonekana bwino kwa mzimu oela ndi kwathu usaika pakati panu katundu wa ukulu kupitilila yaya yali ya lamulo. 29Kuti mng'anamuke kuchoka kuvinthu vichoka kwa chifani mwazi vinthu va kuphedwa ndi uhule ngati simujhiike kwa kutali ndi vinthu ivi siikale bwino kwanu zikomu.''30Chimwecho basi umodamwazidwila adachikila kuantiokia pamalo posonkhanicha msonkhano pamojhi adafikicha kalata. 31Yapo adaisoma adasangala kwa chifuko cha kwaathila mtima. 32Yuda ndi sila ndi olosa wadaathila mtima abale kwa mau yambili ya kaathila mphavu.33pamolo pakukhala nyengo yakuti kumeneko umoanda mwaziduiila kwa mtendele kuchokela kwa abale yaoadatumidwa. 34nampho iaonekana bwaino sila kukukhala kumweke . 35nampha paulo ndi wina yao adakhala kuaantiokia pamojhi ndi wiina ambilinyiyala adayaluza ndi kulalikila maula ambuye.36pambuyo pa siku za kuti paulo wadakamba kwa baranaba ndi tijhibuala chapano ndikwaendela achabale pakati pakila mujhi yapo talalikila mau la ambuye kwa kwaona umo ali. 37barnaba wadafuna kumtenga pamojhi nao yahana uyowadatanidwa marko. 38nampho paulo wadaganizila sati buino kumtenga marko uyowadaasia kumeneko kupamfilia ndikela nao kunchito .39pothela padachokela kuchuchana kwa kukulu kwa chimweko adapatulana ndi arnaba wadamtenga morko ndi kunyamuka kwa. sitima mbaka kukipro. 40nampho paulo wadamsankhula sila ndi kuchoka pamalo popachidwa ndiachabale pakati pa mwawi wa amuye . 41ndi wadapita kupitila kushamu niwamicha mkanisa.

Chapter 16

1Paulo nae yaphowadajha derbendilystra ndi phenya adalipho ndi ophuzila wathanidwa Timotheo ni mnyamantha uyowadabadwa ndi mamawakiyahudi ambayo ni muumini ndi baba wake mgiriki. 2Wantu wa listra ndi ikonia adamuhakikisha bwino. 3Paulo wadamfuna ili wasafilinae chimwecho adamuthenga ndi kumnthalili kwa chifuko chawayaudi anyiyaoadaliko kumeneko kwani oucheadamjhiwa kuti baba wake nimgiriki.4Yapoadali amaphiutha adaphitila kumaiko kumaiko ndikuchocha maagizo kwa makanisa ili kuyatii maagizo yaya yadalembedwa ndi mitume ndi azee huko kuyerusalemu. 5Chimwecho makanisa yamaimarishidwa katika imani ndi anyiyao adaamini adaongezeka kwa idadi ya kilasiku.6Paulo ndi achanjake adaphita Filigia ndi Galatia kwani Roho wa Mulungu wadakhaniza kuhubiri mau kumeko kujimbo la Asia. 7Yapo adakhalibia kimisia ada Yesu kuphintha Bithiania nampho roho wa Yesu wadakhaniza. 8Kwa chimwecho adaphita kumisia adaja mpaka kijiko Troa.9Maono yadamchokela paulo makedonia. 10Paulo yaphowadaona maono mara adajhiandaakuphita makedonia ndiwajhwa kuti mulungu waanthitana kuphintha kuwahubilia injili.11Chimwecho nthidachoka kuchoka troa adaphita moja kwa moja kwa moja samothrake ndi siku iyodachata adafika kujikolaneopali. 12Kuchoka pamenenthidaphita filipi ambaphonimoja ya majhiko ya makedonia jhiko muhimuu kupitila wilaya ndi utawala wakinimi ndi tidakhala siku kadhaa. 13Siku ya sabato tidaphita kubwalo kwa chicheko kwa njila ya mchinje sehemu ambapo thidaganizila sikukhale pamalo pochitila maphephelo tidakala phanchi ndi ndikukamba ndi anyazimai anyiyaoadaja pamoji.14Wamkhazi mmoji watanidwa lidia ugulicha mazambarau kuchokela katika muji wa tiatira mwene wamamuyamika mulungu wadativechelo ambuye adamchakula mtima wake ndikuika maanani mau yadakambidwa ndi Paulo. 15Pambuyo pakubatiza iye ndi nyumba yake yonche adathondoza wadakamba ''ngati mwaniona kutiine ni oaminika kupitila ambuye basi ndikuthozani mulowe ndi khukala kwanga'' wadathuthoza kwabasi.16Ikakala kuti yapotidali timaphita phamalo pa maphemphelo wamkazi mmoji uyowadali ndi pepo la utambuzi wadapezana nafe wadampelekela ambuye wake faida ya mbili kwa kubuni. 17Wamkazi uyu wadamchata Paulo pamoji ndi ife ndi watimbakelele ndi kukamba ''anyiyawa wachimunaniatumikiwa mulungu wali wamkulu anyiyao watangazila anyiimwe ukhani ya uokovu. 18Wadachita chimwecho kwa siku za mbili nampho wa kakhala waiphichidwa ndi vichoto chimecho wadanganamuka kumbuyo ndi kumkambila pepo ''nikulamu la kwa jina la Yesu umchoke mkati mwake'' naye wadachoka ndi kumsia mara kamoji.19Achaambuye wake yapoadaonakuti tumanila faida yao lachoka adagwila Paulo ndi sila ndi kwakweketa kusokoni mbale ya achinawene olamula. 20Yapoadafikacha kwa mahakimu adakamba ''anyiyawa wachimuna ni wayahudi ndi achiticha fujho ya ikulu kupitila mujhi wanthu. 21Ayaluza vinthu ambavo osati sheria ife kuyala ndilo walakuyachta ngati warumi.''22Guru lidang'anamukila kumbuyo Paulo ndi Sila, mahakimu mahakimu adang'amba nchalu zao ndi kwa vula ndi kwaramula atyapidwe viboko. 23Pambuyo pakuwatyapa viboko vambili adatayakugereza ndi kwaramula askari wa gereza kuwalinda bwino. 24Pambuyo polandila maramulo yaya, askari agereza adataya katika chumba cha mkati mwa gereza ndikwamanga myendo yao.25Nyengo ya usiku wa manane, Paulo ndi Sila adali amaphempha ndi kuimba nyimbo za kumtuza Mulungu, uku wafungwa wina amavechela. 26Gafra lidachokela tetemeko lalikulu ndi misingi ya gereza idatingizidwa, vicheko va gereza vidachakluuka ndi minyororo ya afungwa yonche idalegea.27Mlonda wa gereza wadauka kuchokela kulitulo ndi waona vicheko vonche vagereza vachakulidwa; kwachimwecho watenga upanga wake chifuko wamafuna kujiwa kwa ndande wadaganiza omangidwa onche adathothawa. 28Nampho, Paulo wadatimba kelele kwa sauti ya ikulu wadakamba, "siudajipweteka kwa ndande thaonche tili pamalo pano."29Mlonda wa gereza wadaphempha taa zipelekedwe ndi wadalowa mkati mwa gereza kwa chisangu, ndi watentemela ndi kuopa, wadagwela Paulo ndi Sila. 30Ndi kwachocha kubwalo kwa gereza ndi kukamba, "olemekezedwa, nichite chiyani chiyani ili nipate kuokoka?" 31Nao adamkambila, "mwamini Ambuye Yesu nawe siuokoke pamoji ndi nyumba yako."32Adakamba mau la Ambuye kwake, pamoji ndi wanthu wonche kukomo kwake, 33Mlonda wa gereza wadatenga usiku uuja ndi kwasambiza sehemu izoadapwetrekedwa, iye pamoji ndi wantu akukomo kwake adabatizidwa kamoji. 34Wadapeleka Paulo ndi Sila kukomo kwake ndi kuwapilila chakudya. Nae wadali ndi chisangalalo chachikulu pamoji ndi akukomo kwake kwa chifuko adamwamini Mulungu.35Yapo idali usana, mahakimu adapenkhani kwayujha mlonda wa gereza adakamba, "Alamuleni anyiwajha wantu ajipita." 36Mlonda wa gereza wadamjiwicha Paulo pakati pamalo yaja yakuti, "mahakimu apekankhani nilamule muchoke; kwachimwecho machokani kubwalo ndi mjipita kwa mtendele."37Napho Paulo wadakambila, "adatimenya pahadharani wanthu ambao ni Warumi bila kutihukumu ndi adalamula kutitaya kugereza alafu chipano afuna kutichocha kwasi? Palibe siigozeka, nao achinawene aje kutichocha pamalo pano." 38Alonda adajiwicha mahakimu pakati pamau yaya mahakimu adaopa sana paja adajiwakuti Paulo ndi Sila ni Warumi. 39Mahakimu adaja ndi kwatondoza achoke ndi yapo adachocha kubwalo kwa gereza, wadaphempha Paulo ndi Sila achoke kubwalo kwa muji wao.40Kwachimwecho Paulo ndi Sila adachoka kubwalo kwa gereza adapita kukomo kwa Lidia. Paulo ndi Sila yapoadaona abale, adatila moyo ndi potela kuchoka katika muji umeneo.

Chapter 17

1Ni yapo adapita miji ya Amfipoli n Apolonia, adafika hadi muji wa Thesaonike ambao udali ni sinagogi la Wayahudi. 2Ngati umoili kawaida ya Paulo, wadapita kwao, ni kwa muda wa siku zitatu za sabato wadakambana nao juu ya malembo.3Wadali kwavunukulila malembo ni kwaelekezo kuti idambidi Mpulumusi wazunjidwa ni pambuyo kuhyuka nchho kuchoka kwa akufa. Wadakambila, uyu Mpulumusi nikukambilani nkhani zake ndo olamicha. 4Baazi ya wayahudi adavomela ni kuungana ni Paulo ni Sila, pamoji ni Wagiliki akumjiwa Mulngu, anyamame ambili adang'anamuka ni kundi la likulu la wanthu.5Nampho akumoji Wayahudi adakulupalila anyiyao ajala nchanje, adapita kumsika ni kwatenga baazi ya wanthu oipa, adakusanya gulu la wanthu pamoji, nikusababisha vulugu kumjini, baadae adaivamia nyumba ya Jasoni ni afuna kwagwila Paulo ni Sila dala kwapeleka pachogolo pawanthu. 6Nampho yapo wadakosa, adamgwila Yasoni ni baazi ya chabale wina ni kwapeleka pachogolo pa maofisa amuji, abula pokoso "anyiywa wachimuna aling'anamula jiko afika mpaka kunoncho." 7Wachimuna anyiyawa akaribishidwa ni Yasoni awananga lamulo la Kaisari, akamba kuli mfumu mwina watanidwa Mpulumusi.''8Unyinji wa maofisa amuji yapo adavela vichito vimenevo, adajalidwa ni kuopa. 9Baada ya kuti atokala atenga ndalama ya mbili ya kulindila kuchokakwa Yasoni ni wina, wadasia apite.10Usiku uja achabale adamtuma Paulo ni Sila Beroya. Ni yapo adafika kuja adapita katika sinagogi la Wayahudi. 11Wanthu anyiwaja adali ali ni kuelewa kwa mbili kuliko anyiwaja wanthu Akuthesalonike kwa ndande adali ajiandaa kulilandila mau kwa njelu zao, ni kuzuzumila malembo kila siku dala kuona ngati mau yanenedwa yali chimwecho. 12Kwa icho ambili wao akulupalila, akakalamo wachiazi ali ni uwezo waukulu wa Kigiriki ni wachimuna ambili.13Nampho Wayahudi ni Wathesalonike adagundua akuti Paulo watangaza mau la Mulungu Kuberoya, adapita kumeneko ni kukwinjizila ni pamwepo kuyambicha ndeo kwa wanthu. 14Kwa nisanga, achabale ampeleka Paulo kwa njila ya nyanja, nampho Sila ni Timotheo adakala pampaja. 15Anyiwaja achabale adampeleka Paulo adapita nae mpaka Kuathene. Yapo adamsii Paulo kumeneko, adalandila malangizo kuchoka kwake kuti, Sila ni Timotheo aje kwa iye kwa chisanga umo ikozekanila.16Ni nthawi niwalindilila kumene Kuathene, mtima wake udadandaulichidwa mkati mwake kwa umo wadaonela muji umo wati kujala. 17Chimwecho adakambilani katika nyumba ya Mapemphelo ni Wayahudi anyiwaja amjiwa Mulungu ni kwa anyiwaja onche wazana nao kila siku kumsika.18Baazi ya wanafalsafa Awaepikuleo ni Wastoiko adamsendelela. Ni wina adakamba, "ni chiani icho wachikamba uyu mkambaji wamng'ono?" Wina akamba, "ionekana walalikila nkhani ya Mulungu mlendo," Kwandande walalikila nkhani ya Mpulusi ni kuhyushidwa.19Adamtenga Paulo nikumpeleka Areopago, amakamba, "tikoza kujiwa yaya mayaluzo yampya yayo uyakamba?" 20Kwa ndande upeleka vichito va mpya katika makutu yatu. Kwa icho tifuna kujiwa yaya mambo yali ni mate yanji?" 21(Ni wanthu onche Akuathene pamoji ni alendo alipo kwao, atumia muda wao ata katika kukamba ni kuvechela juu ya jambo lampya.)22Kwa icho Paulo wadaima pakatipakati pa wanthu Areopago ni kukamba, "Anyiimwe wanthu Akuathene, nione kuti anyiimwe ni wanthu adini kwa kila ntundu, 23Kwani katika kupita mwanga ni kupenyelela vinthu vanu va mapemphelo, napenya mau yalembedwa kumadhabahu yanu yakamba, "KWA MULUNGU WAJUWIKANA." Chimwecho basi uyo mumphemphe bila kujiwa, ndiiye nikujuwishani anyiimwe.24Mulungu uyo wakonja jiko, ni kila kanthu chili mkati, pakuti ni Ambuye akumwamba nipanchi, siakoza kukala katika nyumba nyumba zakonjedwa kwa manja. 25Ni pia siwatumikilidwa ni manja ya wanthu kuti wafuna chinthu kwa nyiio, kwani iye mwene wapacha wanthu umoyo ni pumzi ni vinthu vina vonche.26Kupitila munthu mmojhi, wadaita maiko yonche ya wanthu akala pamwamba pa mphumi ya jhiko ni wadaikila nthawi ni malile katika malo akala. 27Kwa icho afunika kumfunafuna Mulungu, ni yapasa amfikile ni kumpata, ni kwa uhakika siwali patali ni kila mmoji watu.28Kwa iye tikala, tienda ni kukala ni umoyo watu, ngati uja otunga wanu mmoji wanu wa shairi yapo wadakamba, "tiliobadwa wake." 29Kwa icho ikakala, ikakala ife ni obadwa a Mulungu, siifunika kuganizila kuti Uungu ni ngati dhahabu, au shaba, au myala, chosepedwa chasepedwa kwa ubwino ni maganizo ya wanthu.30Kwa icho, Mulungu wadakalila chete nyakati zijaza kuwewela, nampho saino walamua wa nthu onche kila pamalo apate kupempha. 31Ili kwa ndande waika siku iyo siwalamule jiko kwa zene kwa munthu uyo wadamsankha. Mulungu wadachocha uhakika wa munthu uyu kwa kila munthu paja wadamhyusha kuchoka kwa akufa.32Ni wanthu Akuathene yapo adavela nkhani ya kuhyushidwa akufa, wina wao adamtukana Paulo, ila wina adakamba, "tikuvechelancho kwa nkhani ii" 33Pambuyo pake, Paulo wadasia. 34Nampho baazi ya wanthu aungana nae adakulupalila, wakakalamo Dionisio, ni wamkazi watanidwa Damari ni wina pamoji nao.

Chapter 18

1Baada ya vinthu vimenevo, Paaulo wadachoka kupita Kukorintho. 2Kumeneko wadampata Myahudi watanidwa Akwila munthu wa kabila la Ponto, iye ndi mkazake watanidwa Prisila adaja kuchoka kumeneko Kuitalia, kwa chifukwa Klaudia wadalamula Wayahudi onche achake kurama, Paulo wadaja kwao; 3Paulo waishi ndi kuchita nchito nao kwani iye wachita nchito ilingana ndi anyiiwo anyiiwo adali ndi akonja mabanda.4Paulo wadapatakaz nao mkati mwa nyumba mwa mapemphelo kila siku ya sabato. Wadaanyengezela Wayahudi pamoji ndi Wagiriki. 5Nampho Sila ndi Timotheo yapoadaja kuchoka Kumakedonia, Paulo wadasukumidwa ndi mzimu kwaalangiza Wayahudi kuti Yesu nde Kristo. 6Nyengo Wayahudi amamkanila ndi kumpepula, mchimwecho Paulo wadakung'untha nchalu zake pachogolo pao, ndi kwaambila, "mwazi wanu ndi ukale pamwamba pa myutu yanu mwachinawene, ine ndilibe kosa. Kuchoka saino ndi kuendekela, ndachata apajiko."7Mchimwecho wadachoka paja wadapita kunyumba ya Tito Yusto, munthu uyowamgwadila Mulungu. Nyumba yake ili karibu ni nyumba ya mapemphelo. 8Krispo, wamkulu wa nyumba ya mapemphelo pamojindi wanthu amnyumba mwake adamkulupalila Mbuye. Wanthu ambili wa Korintho yapoadamvela Paulo ndi wakamba adaklupalila ndi kubatiza.9Ambuye adamkambila Paulo usiku kwa njila ya maroso, "usidaapo, nampho kamba ndi usidakala kachete. 10Kwani ine ndi pamoji nawe, ndi palibe uyasiwaese kukuchita choipa, pakuti ndili ndi wanthu ambili mkati mwa muji uu." 11Paulo wadakala kumeneko kwa muda wachaka chimaji ndi myeezi sita ndi wayaruza mau la Mulungu mkati mwao.12Nampho Galio yapo wadachitidwa kukala olamula wa Akaya, WAyahudi adaima pamoji asagwilizane ndi Paulo ndi kumpeleka pachogolo pa mpando wa lamulo. 13Adakamba, "munthu uyu wanyengezela wanthu amgwadile Mulungu kumbuyo ndi ramulo."14Nyengo Paulo yapo wamafuna kukamba, Galio wadaakabila Wayahudi, "anyiimwe yahudi, ngati idakankala kasa au kuwananga, idakakala uzene kuwapotela nchito. 15Nampho kwa chifuwa ndi mafunchidwe, yayo yahusu mau ndi majina, ndi lamulo la, Basi lamujlani anyaimwe mwachinawene sindikumbila kukala olamula kwa makambidwe ya vichito vimenevo."16Galio wadalamula achoke pachogolo pa mpando wa lamulo, 17Mchimwecho, adamgwila Sosthene, wamkulu wa nyumba ya mapemphelo, adambula pachogolo pa mpando wa lamulo. Nampho Galio siwadaganizila icho adachichita.18Paulo, baada ya kukala paja kwa nthawi ya Itali, wadaasia achaabale ndi kupita kwa chombo siria pamojin ndi Prisila ndi Akwila kabla ya kuchoka padooka, wadameta chichi lake lonche kwani wadalapa kuti osunga lamola. 19Yapo adafika Kuefeso, Paulo wadamsia Prisila ndi Akwila paja, nampho iye mwene wadalowa mnyumba ya mapemphelo kufotokozelana ndi Wayahudi.20Yapo adamkambila Paulo wakale nao kwa nyengo ya yitari, iye wadakana. 21Nampho wadachoka kwao, wadaakambila, "sindibwelencho kwanu, ikakala ndi kwa chikondi cha Mulungu." Baada ya pamenepo, wadacheka kwa chombo kuchoka Kuefeso.22Paulo yapatula Kukaisaria, wadakwela kupita Kusamaria kunyumba ya mapemphelo ya Kuyerusalemu, ndeyapo wadachika panchi kwa anyumba ya mapemphelo ya Antiokia. 23Baada ya kukala kwa nthawi paja, Paulo wadachoka kupita kumalo kwa Galatia ni Frigia ndi Kwaatila mtima opuzila onche.24Myahudi mmoji watanidwa Apolo, uyowadabadwa kumeneka ku Alexandria, wadaja Kuefeso wadali ndi uzene mkati mwa kukamba ndi bidii mkati mwa malembedwe. 25Apoli wadaelekezedwa pakati pakuyaruza kwa Ambuye kwa chifukwa umowadali ndi bidii mkati mwa mzimu, wadakamba ndi kuyaluza kwa uzene vichito vimuhusu Yesu, nampho wadaujiwape ubatizo wa Yohana. 26Apolo wadayamba kukamba kwa mphavu mkati mwa nyuma ya mapemphelo. Nampho Prisila ndi Akwila yapoadamvela, adachita ubwenji naye ndi wadaelezea pamwamba pa njila ya Mulungu kwa uzene.27Yapo wadakhumbila kuchoka kupita kwa Akaya, achaabale adamtila mtima ndi kwalembela karata opuzila anyiyawo ali ku Akaya ili apate kumlandila. Yapo wadafika kwa neema wadatangatila sana anyiwaja adakhulupalila. 28Kwa mphavu zake ndi njeru, Apolo wadaazidi Wayahudi pawazi ndi walangiza kupitila malembedwe ya kuti Yesu nde Kristo.

Chapter 19

1Idali Apoolo yapowadali ku Korintho, ndi Paulo wadaendela maiko ya pamtuna ndi kufika pa mujiwa Kuefeso, ndi wadaasumana omphumira akuti kumeneko. 2Paulo wadaakambila, bwanji mudalandila mzimu oyera yapo mudakulupalila?'' Adamkambila, noto, sitinakhoze kuvelapo za mzimu oyera.''3Paulo wadakamba chipano anyiimwe mudabatizidwa bwanji? Adakamba tidabatizidwa ndi Yohana. 4Nampho Paulo wadayankha, "Yohana wadaabatiza ubatizo wakulapa, wadaakambila anyiwajha wnthu kuti afunika kumkhulupilila yujha iye wakadajha pambuyo pake kuti ndi Yesu."5Munthu yapoavela nkhani iyi adabatizidwa mjhina la Yesu. 6Ndiidali kuti Paulo yapo wasanja manja, Mzimu Oyera wadachikila ndi adaba kukamba pa mikambo yolekanalekana ndi kulalika mau ochokela kwa Mlungu. 7Pamoji adali wachimuna khumi ndi awili.8Paulo wadalowa mnyumba ya maemphelo ndi kuyamba kukamba wadakhala pa myezi itatu. wamakhambana ndi wanthu ndi kwaguza wanthu pa nkhani ya ufumu wa Mulungu. 9Nampho Ayahudi wina adali ouma mitima ndi osafuna kukhulupilila, adayamba kukhamba mau yoipa pakati pa njila ya Kristo pamaso pa gulu. Nampho Paulo wadasiyana nao ndi kuwasankha okhulupilila patali ndi anyiio wadayamba kukamba masiku yonche mnyumba ya Tirano. 10Izi zidaendekela pa zaka ziwili anyiyao amakha Kuasia adavela mau la Ambuye, onche Ayahudi ndi Ayunani.11Mulungu wamachita vichito vavikulu kujela manja ya Paulo. 12Kuti ingakale odwala adalamichidwa, ndi mizimu yoipa idaachoka, yapo adatenga chitambaya ndi nchalu zochoka mthupi la Paulo.13Nampho padali ndi Ayahudi ochocha mizimu yoipa adaenda enda kujela malo yaja adatumikila jhina la Yesu pa ndande zao achinawene ndi kuakambila anyiwaja adali di mizimu yoipa, kukamba ndikulamulani muchoke pa jhia la Yesu uyo Paulo wamlalikila. 14Adazichita izi adali wana asano ndi awili wa ankulu wa nchembe Wachiyahudi, Skewa.15Mizimu yoipa idayankha, Yesu ndi mzindikila ndi Paulo ndi mzindikila nampho anyaimwe achiyani? 16Ujha mzimu oipa mkati mwa munthu udalumphila ochocha mizimu yoipa ndi kuwamenya ndeyapo adathawa kuchoka mnyumba muja ali maliseche ndi apwetekedwa. 17Izi zidajikana ndi wonche, Ayahudi ndi Ayunani, yawo amakha kumeneko ku Efeso ndi adali ndi mantha kupunda, ndi jhina la Ambuye lidapambana kulemekezeka.18Akristo ambili adaja ndi kulapa ndi kulangiza vichito vao voipa ivo adachita. 19Ambili amachita ung'anga udasonkhanicha vikalakala vao, ndi kubucha moto pa maso pa waliyonche, nyengo anyaio adawelenga mtengo wa vinthu vija, idali vibanthu makumi asano. 20Kwaicho mau la Ambuye lidakula kupunda.21Paulo kukwanicha nchito yake kuja ku Efeso Mzimu udamchogoza kupita ku Yerusalemu kujela ku Makedonia ndi ku Akaya; wadakamba pambuyo pokala kua, ndifunika kupita ndi ku Rumi. 22Paulo wadatumiza omphunzira ake awili kupita ku Makedonia. Timotheo ndi Erasto yao amamthandiza. Nampho mwene wake waakhala ku Asia pa kanthawi.23Nyengo imeneyo padachokela chipolowe cha chikulu ku Efeso pakati pa njila ija. 24Wanchito za siliva mmojhi jhina lake Demetrio, wadakonja timafanizo la ndalama ya mulungu Diana wadapeleka malonda yayakulu kwa anchito wake. 25Kwaicho wadasonkhanicha anchito ija ndi kukhamba, olemekezeka mjiwa kuti pa malonda yaya ife tipheza makobili ya mbili.26Muona ndi kuwela kuti, osati pano Paefeope, nampho pafupi Asia yonche, uyu Paulo waaguza wanthu ambili ndi kuang'anamula wakamba kuti palije milungu iyo yachitika ndi manja. 27Ndi osatipe malonda yathu yalimmavuto, siyakhale siyafunikancho, nampho nyumba ya Mulungu wamkazi wali wamkulu Diana siwaoneke walije mate, ndi wakhoza kuluza ukulu wake iye Asiya ndi jhiko amphemphera.''28Yapo adavela izi adajalidwa ndi mphwayi ndi kuchita mapokoso ndi kukamba kuti Diana wa Kuefeso ndi wamkulu. 29Muji wonche udajala chisokanizo, ndi wanthu adatawa pamoji mbwalo la masewela adagwilidwaoyenda njila anjake ndi Paulo, Gayo ndi Aristarko amechokela Kumakedonia.30Paulo wamafuna kulowa mgulu la wanthu na mpho omphuziza adamchekeleza. 31Akulu aboma la Asia akumoji adali mabwenji lake adampelekela utenga wamphamvu kumuphempha wasadalowa mbwalo la masowela. 32Wanthu akumoji amakamba ichi wina chija, ndande gulu la wanthu lidali lsokanizika, ambili samajiwe ndande chiyani adali pamoji.33Ayahudi adamtulucha Iskanda kubwalo kwa gulu la wanthu ndi kumkweza pamwamba pa maso pa wanthu. 34Nampho yapoadajiwa kuti iye ndi Muyahudi wonche adachita mapokoso pa mau limoji pa nthawi, "Diana ndi wamkulu wa Kuefeso."35Pambuyo pa mlumbi wa mujiwo kuakalicha wanthu chhete, wadakamba, "anyiimwe waachimuna Akuefeso yani siwajiwa kuti muji uno wa Efeso ndi wasunga nyumba ya Diana wamkulu ndi ija piicha idagwa kuchokela kumwamba?" 36Pakuona kuti izi sizikhozekana, tifunika kukhala chete ndi msachita chilichonche msanga. 37Mate yake mwatana wanthu anyiyawa wakuakulu anchembe osati ankhungu a nyumbna ya Mulungu ndi osati onyoza Mulungu wathu wamkazi.38Kwaicho ngati Demetrio ndi anchito ali pamoji ndi iye ali ndi milandu pakati pa munthu waliyonche, bwalo la milandu lilipadanga ndi olamula alipo apelekedwe. 39Ngati iwe ufuna chilichonche pa vinthu vinjake zikaveka ku msonkhano. 40Uzene kuti tili pipa pakuimbicha mlandu pakusokaniza siku la lelo, palije ndande vuto ili ndi sitikoza kujikambilla. 41Wakhate kukhamba yaya wadaakamba wanthu ajipita.

Chapter 20

1Pambuyo potha phokoso, Paulo adatanisa ophunzila waja, nawalimbitcha mtima. Ndipo adawalaila iwo adachoka napata ku Makedonia. 2Adayendela madela akumeneko, nalimbisa mtima wanthu ndi mau ambili pambuyo adapita ku Grisi. 3Anakakhalako miyezi yitatu, pamene adali pafupi kupita ku Silia pachombo Ayuda anachita chiwembu. Pamenepo adaganiza zopita njira ya ku Makedonia.4Adampelekeza Sopatre mwana wa Piro, w ku Berea; Aristarko ndi Sekondo a ku Tesalonika, Gayo wa ku Deribe; Timotheo ndi Tikiko ndi Trofimo a ku Asia. 5Koma wanthu adatha kusogela ndi adali akulindilila huja Tirowa. 6Kwa panjila ya panyanja kufikila ku Filipi, pambuyo pa masiku amikae yapande choupisa ndi masiku asano tidafikila kuja ku Tiroa. Tidakala kumeneko masiku saba.7Pa siku loyamba la sabato, tidasonhana kuti tidye mgonelo, Paulo adakamba ndi anthu pakuti ankayembeza kupita umawa wake, adapitariza kukambawo mpekana pakati pa usiku. 8Panali nyali zambil mchipinda cha golofa umo tidasonkana.9Pawindo panali mnyamatawina zina lake Utiko amene adalema ndi liturolamphanivu. Ata Paulo pamene amahubili amunthawi yaitari, nnyamata uyu adali atagona, adagwa pasi, kuchakela kumwamba kwa golofa aje katatu ndi adatondoledwa atefakale. 10Kona Paulo adasika pasi naziponya pamnyamatayo namkhuambatrira, "ndi musanivutike pakuti ali moyo."11Ndipo adakwela kugholofa ndi anamenya mkate adadya. Pambuyo poamba ndi kwo mzithawa yayotari, mpakana umawa adanyamaka. 12Ndipo anthu wajaadamutenga mnyamata uja wali wamoyo ndi montche akondwela kupunda.13Ife tidasogolela kukakwela chombo kupita ku Aso kumene tidaganizila kukamtengeka Paulo, iyeadakoza chimwechi chifukwa adafuna kupita pamtunda. 14Pamene adafika ku Aso, lidamweza mzisitima tiapita ku mutulene.15Pambuyo pake ife tidachoka kumeneko ndi siku la kawili lidafika mbali ya ya kawiri ya chilumba cha Kio. Siku losatira tidafika chilumba cha samo ndi umawa wake lidafika muji wa Mileto. 16Paulo dasimikiza zolambalala Efeso, kuopa kutaya nthawi kujiko la Asia; aankatulumila kuti ngati kotheka akathole ali ku Yerusalemu pa siku la Pentekosite.17Kuchoka ku Muleto adaluma wanthu mpaka Efeso ndi kwatana akulu ampingo. 18Pamene adafika kwa iye adawakambila imwe mwawene mujiwa kuyambila siku yoyamba nidaponda pano pa Asia mmene nidali kwanu nthawi yonche. 19Nkamtumikila Ambuye anozichepecha kupunda pakati pa zowawa ndi zomvuta zimene zidandogwela chifukwa cha viwembu va Ayuda. 20Mujiwa kuti sindinakubisileni kanthu kalikonse koti nkuthandizen. Ndidakuhubilani nde kukuyeluzani poyela ndi mzinyumba zanu. 21Ayuda ndi Agriki omwe ndidapempha kolimba kuti atembenukile kwa Mulungu molapa ndi kumakhuupilila Ambuye wathu Yesu.22Ndi sophano penyentehani ine ndikunivemeleza Mzimu Oyela kupita ku Yerusalemu, amene sindimaziwa zimene zikachitela ine kumeneko. 23Kama pakuti Mzimu woyela akundichitila umboni ine, kuti mudzi uliontche akukamba kuti zowana ndi zopwetika ndizomene zikundidikila. 24Hama sindiganiza zamayo wanga, ngati ndi wamitengo wapatari kwa ine, malinga ndikamaliza nchito yanga ndi utumiki uwo Ambuye Yesu adandipasa, kuti kulalika poyela uthenga wabwino mena za kukoma mitima kwa Mulungu.25Tchapano ndijiwa kuti ununu nzonche amene ndidaklalikilani za ufumu wa Mulungu, semuzaonaso nkhope yanga ai. 26Chifukwa chake ndikuuzani monenesa lero, kuti ngati ena mwa inu atayike, izo nzake, une ndi libe mlandu. 27Pajatu sindidakubisileni kanthu ai koma ndiolakulalikilani vontche vamene Mulungu afuna.28Mzimu Woyela adakuikani kuti mzipenyelela kanisa lyonche, nchipano mzisande mwene, ndi kusandaso kanisa. Wetani nkhos za kanisa la Ambuye, uo adaombola ndi mwazi wao. 29Ndijiwa kuti ndakazachoka ine, pazalowa momblu yowopya pakati panu, iyo sizaelekelela nkhasazo. 30Ngakhale pakati panu pomwe pazauka ena okamba vamtila ndi kumnyanga ophunzila kuti awasate.31Imwe khalani maso, kumbukilani kuti pa zaka zitatu ubana ndi usiku sindidaleke kukuyeluzani aliyenche mwa inu ndi misozi. 32Mchiwechi sopano ndikukuikani mmanja mwa Mulungu, azaze yake woonesa kukoma mtima wake akusungeni bwino. Mauo ali ndi mphamvu za kukulisa mpingo, ndi kukupeni madaliso yontche yayo Mulungu akusungulani wanthu wake.33Sindakolakhumbile ndarama kapena zomvala za munthu aliyetche ai. 34Imwe mjiwa kuti manja angawe adagwila nchito kuti ndipeze vinthu vimene ine ndi azangavematisowa. 35Pa vontche ndakupatchani kuti pakugwila nchito kolimba, chimwechi olimba, tiyenela kuthandiza oofoka. Kumbukilani mau a Ambuye Yesu akati kupesa koposa kulandila.36Yapo Yesu adakamba vimenevi adagwada pesi namphepete nawo pamoji ena wotche waja. 37Wontche adalire kupunda. Adamkhumbatira pauloyo nam'busu na mulayilana naye. 38Makamaka adachita lisungu chifukwa cha mau yake yej onene kuti noo iwo sazamuanatcho nhope yake pambuyo adamupelekeza ku chombo.

Chapter 21

12Ntawi imene tidaiana nao ndi tilipaulendo mnyanja, tidfika moja kwa moja mkati mwa muji wa kosi ndi siku lakawila lake tidafika mmoji wa Rodo, ndikuchokela kumeneko tidafika mmuji wa Patara. Yapo tidapeza sitima yoyomboka kupita Kufonike, tidakwela ndi kuendekela.3Yapotidafika pachogoro pa chilumba Kipro tidasia janja la kumanjele tida enda mpaka ku Siria tidaika chipumulizi pamoji wasilo chifuko kumeneko ndiko idalisitime ikwe zeke katundu wake. 4Pambuyo pakwaona oyaluzidwa tidakale kumeneko masiku saba oyaruzidwa yawa adakambila Paulo kupitila mtima kuti iye siwaponda ku Yerusalemu.5Atapamenepo tidamalze masiku yaja ife tidachoka tidapita ulendo watu. Onche pamoji ndiocha akatu ndi wane watu adatipelekeze pakati panjila zetu tidaturuka kubwalo. Kubwalo kwa muji pambuyo tidagw maomono mpepete mwa nyanja, tidapempela, tidelailana ndi waliyenche. 6Tidakwela sitime ukunaoncho atabwela mmiji mwaoncho.7Atayapo fido tela uleudo watu kuchokele kutilo tide fika kutolemai paja fide conjelawa ndi abale ndi kukale nao siku limoji. 8Mawalake fide choka fide pita kukaisana ife tidalowa mnyumba ya Filipo olalikila mau la Mulungu uyo wadali mmoji wa anyi waja saba nafencho tidekale pamoji naye. 9Muntu uyo wadali ndi ana mwali anai achamene adali osabalapo acha amene adaleta.10Pambuyo pakukala kumeneko kwa masiku yakuti wadachika kucho kela Kuuyahudi orofa mmoji watanidwa Agabo. 11Iye wadaja kwatu ndi wadatenga lamba la Paulo chifuko wadaji manga miendo ndi manja yake mwenewake ndi kukamba, Mzimu Woyera wakamba chimwechi, "Wayahudi wa Kuyerusalemu sioa mmange muntu wamgwilirila lamba ili naoncho simpache mmanja mwa wantu ajiko."12Yapo tidavela nkani izi ife ndiwa amene amalama malo yaja tidampembeza Paulo siudakwela kupiita Kuyerusalemu. 13Nde pamene wadayanka mchita chiyani mulela ndikuti dula mtima? Chifuko chamate ndili tayari usati kumangidwa chabe nampo kutera komweko Kuyerusalemu chifuko chajiona la Bwana Yesu. 14Chifuko Paulo siwadafune kunanizidwa, tidasiane ndikukamba, "basi chikondi cha Mulungu chichefike."15Pambuyo pama siku yameneyo, tidatenga matumba yatu ndifita kwela Kuyerusalemu. 16Moochepa mwa oyanzidwa wake kuchokela Kukaisaria naonche ada chatano nafe. Adaja naye mvute mmoji watanidwa Mnasomi muntu wa Kipro oyaluzidwa wakalemmene tide kala naye.17Yapo tidafika Kuyerusalemu abale adati landila kwa chikondi. 18Siku la kawili lake Paulo wadapita pamoji nafe kwa Yakobo, ndikuwazee wonche adalipo. 19Pambuyo pa kuwalonjela wada apacha nkani imoji mwaina ya nkani zimene Mlungu wadachita mkati mwa maiko kwa kuptila chitandizo chake.20Ntawi yapo adavela yameneyo anamkwezeka Mulungu, ndiada mkambila, "upenya abalewako kuli wantu wa anyinji akurupalila mkati mwa Wayahudi anyio wonche ali ndi chikurupalilo chogwila lamulo." 21Akambilidwila kuchatana ndi iwe kuti uyaluza Wayahudi akale pakati miko kusiane ndi kuti wakambole kuti si adeatandize achi wana wao ndi siadafunafuna mwab wao wakale.22Ifunika tichite chiyani? Kapena pake kapena siavele kuti iwe wafika. 23Mmwemo chita chija ifeti kukambila chapano tili ndi wantu anai ameni aika pangano. 24Atenge achiwantu yawa ndi ujichuke wmwene pamoji ndi anyaiwo ndiuwa lipile vonche vimene atudikila dala kut akoze kumeta mitu yao mmwemo waliyenche nkani zimene akambidwa kupisila uwe ndi zaunami siayaluze kuti iwe nawencho uchata malamulo.25Nampo kwa nkani za wantu ajiko acha amene ali ochatila tidalemba ni kuchocha maagizo kuti afunika kujiika pampepete ndi vinthu vchochedwa chabilokela ndi chiati chapotedwa ndi ajiike pampepete ndi chigororo. 26Ndi pawene Paulo wada atenga waachimuna ndi siku la kawili kujipembeza pamoji ndi anyiiwo wadalowa muhekalu ktangaza chipindi cha siku za kujipembeza mpakane sadaka ichochedwe chifuko cha waliyenche wao.27Siku zimene saba yapo zidawandikile Wayahudi ochepa kuchokela Kuasia adamuona Paulo muhekalu ndi ana kanyinji adakwiya ndi kumkwezela maya. 28Adali ndi ameinya pokoso "wanthu wa Kuiziraeli, mtitangatileuyu nde yuja wa ayalua wanthu pamalo pali ponche nkani zimene zili kumbuyo ndi wanthu, lamulo, pamalo pano sonincho wanjanao Wayunani pakatikaty pa nyumba ya mapempelo ndi kupachita ukazuzu pamalo pano pali malo ya bwino." 29Pakuti poyamba adamuona Trofilo Muefesowali pamoji nao mumuji, naoncho ameaganiza kuti Paulo wadaja naye mmalo mapempelela.30Muji wonche udali ndi walowa pokoso, ndi wanthu adatawa pamoji ndi kumgawira Paulo, adamchocha kubwalo cheko kamoji vidamangidwa. 31Yapo amayesa kufuna kumpa nkani zidamfikila wamkuru wazankondo la ochekeleza Muyerusalemu yonche idalowa mtimbwilikanyo.32Ntawi yomweyo wada atenga azankondo ndi wamkuru wazankondo wadalitamangila guru, ntawi wantu yapo adamuona wanikuru wa zankondo ndi asirikali wake, adasia kumtimba Paulo. 33Pambuyo pake wamkuru wa zaukondo wadamsedelea ndi kumgwira PAulo ndi kulamula wamangidwe vingwe vya chichulo viwili. Wadamfuncha iye ndiyani ndi wachita chiyani.34Wantu ochepa mkati mwa guru amango kambakamba wena akamba ichi wena akamba icho. Pakuti wambile chilichonche kifuko cha yaya mapokoso wadalamula Paulo wapelekedwe nyumba ya malamulo. 35Kusia chimenecho yapo wadafika pa makwelelo wadatengedwa ndi azankondo chifuko chamtimbwilikanyo wawantu. 36Chifuko guru la wantu adamchata ndi adaendekela kubula mapokoso, "mchocheni uyu."37Paulo yapo wamapelekedwa mkati mwa nyumba ya malamulo, "wadamkambila wamkuru wazankondo" ndikoza kukukambila chinthu? Yuja wamkuru wazankodo wadakamba, "bwanji ukamba Kiyunani?" 38Bwanji iwe osati yuja Mmisri poyamba wadachogoze kwakila ndi wadaatenga oukila elfu ne ntengo?''39Paulo wadanena, "ine Muyahudi, kuchokela muji wa Tarso ya Kilikia. Ine ndili mmoji wajiko lojiwika nikukupempani mundilole ndikambe ndi wantu." 40Ntawi wamkulu wazankondo yapo wadampaja lamulo Paulo wadaine pamakwelelo ndikuchocha chilangizo kwa wanthu kwa janja lake, ntawi yapo kudakala kachete kupunda, wadakamba nao kwa Kihebrania. Wadakamba,

Chapter 22

1Abale ndi acha atate wanga vechelani chitetezi changa siniichichite kwanu chipano. 2Ansoghano yapoadavela Paulo ndi wanena nawo kwa Chiebrania adakala chete. Kunena,3"Ine ndi Myahudi, nabadwa mujhi wa Tarso malo la Kilikia nampho nidapata mayaluzo pa mujhi uuni, pamyendo pa Gamalieli. Nidayaluzidwa kulingana ndi njila zene za matauko za atate wantu. Ine ndili ni jhitajhita ya Mulungu, ngati anyiimwe mwawonche umo muli lelo. 4Nidekupwetekani kwa njila iyi mpakana kufai nidakumangani wachimuna ndi wachikazi ndi kukutayani mndende. 5Ata wamkulu wa nchembe ndi midala wonche akoza kuchocha umboni kutinidalandila kalata kuchoka kwaiwo kwa chifuko cha abale li kudameski kwa ine kusafiri kupila kumeneko idali nikupelekeleni wanthu kuyerusalemu kwa njila ijha kuji omangidwa avutichidwe.6Idachovela kuti pajha nidali paulendo kuwandikila ku dameski nyengo za usana chizulumukila ndangalila lalikulu lidachokela kumwamba idayamba kunimulika. 7Nidagwa panchi ndi kuvela mau kunikalubila sauli sauli chifukochanji uvidanda ulicha. 8Nidayankha, "iwe ndi yani atate?" wadanikambila , "ine ndi yesu mnazereti nyo ine umdaulicha.'9Anyiwajha adali ndi ine adaona adangalila, nampho siadavele mau yayujha uyo wadanena ndi ine. 10Nidanena, nichite chiyani, Atate? Atate adanikambila, "ima ndi ulowe Kudameski; kumeneko siukamblidwe kila chindhu ufunika kuchita." 11Sinidakoze kupenya lava ndende ya mwangaza wa dangalila lijha, ndipo nidapita kudameski kwa kuchogo lelendwa ndi manja ya anyiwajha adali ndi ine.12Kumeneko nidakomana ndi mundhu watanidwa Anania wadali mundhu uyo wadagwila matauko ndi mwene kulemekezeka pachogolo pa Wayahudi amakala kumeneko. 13Wadajha kwa ine, wadaima pachogolo panga, ndi kunena, mbale wanga Sauli, upeze kupenya: kwa ntawi imweijha nidamwona.14Adanena mulungu wa Atate watu wakusagula iwe upeze kujhiwa chikondi chake, kumwona yujha mwene chilungamo, ndi kuvela mau yachoka pakamwa pake. 15Kwa ndande siukale mboni kwiye kwa wandhu wonche pamwamba pa yayowayaona ndi kuvela. 16Mmwemo chipano kwa chiyani unilindilila? Ima, abatizidwe, ukachukidwe machimo yako, ndi ulitana jhina la iye.'17Pambuyo pa kubwela Kuyerusalemu, yapo nidali ndinipembhela mkati mwa nyumba yopembhela, idachokela kuti napachidwa maloso. 18Nidamuona niwanikamila chichimichimi uchoke Kuyerusalemu msanga, kwa ndande siavomela umboni waiwe kukuza ine.'19Nidakanena Atate anyiiwo achinawene ajhiwa nidaamang'a mudende ndi lawa menya anyiwajha adakulupalila pa masinagogi. 20Ndi mwazi wa Stefano mmboni wa iwe yapo idamwazika, ine nane nidali naima powandikila ndi kuvomela ndi nidali ndisunga nchalu za anyiwajha adampha. 21Nampho adanikambila, "mapita kwa ndande ine sinikutume upite papatali kwa wandhu ajhiko."22Wandhu adampacha lamulo akambe pamwamba pa maunli. Nampho pambuyo adakuzi mau ndi kunena, "mchoche mundhu uyu pa jhiko; kwa ndande osati zene walame." 23Yapo wadakuza mau ndi kumtangatila vovala volwo ndi kutaya malifumbi kumwamba. 24Jemedali wamkulu wadalamula Paulo wapelekedwe mnyumba, wadalamula wafunchidwe pamwepo ndi watimbidwa vichailo, kuti iye mwene wajhiwe kwa chiyani wadali kumtimbila mapokoso ntundu ujha.25Ata yapowadali ammanga kwa maluzi, Paulo ademkambila yuja akide wada ima kuwandikilana ndi iye, Bwanji ni malinga kwanu kumtimba mundhu wali Mrumi ndi wakali kulamulidwa? 26Yujha akida yapo wavaela mau yajha, wadapita kwa jemadari wamkulu ndi kumkambila kunena' "ufuna kuchita chiyani? Kwa mate mundhu uyu ndi Mrumi."27Jemedari wa mkulu adajha ndi kumkambila, "niambile, bwanji iwe ndi wa mujhi wa Kurumi?" Paulo wadanena, yetu. 29Jemedari wadayankha, "ndi kupitila unyinji za ndalama ndipo ndidapeza." Nampho Paulo adamkambila, "ine ndi Mrumi wa kubadwa." 28Basi anyiwajha adali tayari kupita kumfucha adachoka ndi kumsiya nyeno imweijha. Ndi jemedari naye wadawopa, yapo wadajhiwa kuti Paulo ndi Mrumi, ndi kwa ndande wamwanga.30Siku idachatila, Jemedari wamkulu wadafuna kujhiwa uzene kukuza milandu ya Wayahudi kupunda ya Paulo. Chimwecho adammasula vilunjo vake wadalamula wamkulu wa nchembe ndi bwalo lonche apezane. Adampeleka Paulo panchi ndi kumwika pakatipakati pawo.

Chapter 23

1Paulo wdaapenyesha wanthu a baraza ndi kuakambila, abale wanga ndakala ndikufunila za bwino mbaka lelo pamaso pa Mulungu. 2Wamkulu wa anchembe, Anania wadaalamula anyiwaja adima pafupi ndiiye am'bule kukamwa kwake. 3Paulo wadamkambila, "Mulungu siwakubulelwe, pupa lanyekedwa, wakala unilanga kwa tauko ndi ulamula nibulidwe pasachata tauko?"4Anyiwaja adaima pafupi ndi iye adakamba chimwechi nde umo umtukwanila wamkulu wa nchembe wa Mulungu? 5Paulo wadakamba, "achiabale wanga ine sinidajiwe kuti uyu wamkulu wa nchembe. Pakuti yalembedwa, siukamba kuipa kwa oimilila wanthu wako."6Paulo yapo wadaona pa gulu lija kuli Afarisayo ndi Asadukayo, wadakamba kwa mphavu achiabale wanga ine ndi Mfarisayo mwana wa Mfarisayo, napelekedwa pa koti chifukwa ndikulupilila akufa sahyuchidwe. 7Yapo wadakamba chimwechi ndeo idachokela kwa Asadukayo ndi msonkhano udasweka. 8Ndande Asadukayo akamba kulibe kuhyuchidwa, palibe angelo, palibe mzimu, nampho Afarisayo akamba voncheo vilipo.9Ndeo yaikulu idachokela, akumoji wa olemba wa Afarisayo, adaima ndi kukamba sitidachionechoipa kwa munthu uyu, bwanji, pena mzimu, kapena angelo acheza ndi iye? 10Ndeo idapunda kukala yaikulu, wamkulu wa asirikali wadaopa kuti Paulo angamng'ambeng'ambe kwa icho wadaalamula asirikali wake kulwelela gulu lija ndi kumchocha Paulo ndi kum'bweza mkati.11Usiku udachatila Ambuye adaima pafupi ndi Paulo adamkambila, "usaopa, wanichitila umboni mu Yeruslemu, ndi Kuroma nako ukachocha umboni wanga."12Yapo kudacha akumoji mwa Ayuda adajiikila chileso achinawene kuti sitidya ndi stimwa chilichonche m'baka yapo sitimpe Paulo. 13Kudali ndi wanthu oposa makumi anai amapanga khani imeneyi.14Adapita kw waakulu anchembe ndi kukamba tajiika tawefe mchileso chachikulu kuti, "tisa dadya chilichonche m'baka timpe Paulo. 15Kwaicho baraza limkambile wamkulu wa asirikali wakamtenge waje nayo kwa anyiimwe kuti mkuja kulamula mlandu wake mwawe kuti mkuja kulamula mlandu wake mwa malinga ife tajikonja kumpa wakali osafike pano."16NAmpho mwana wa m'bale wake Paulo wadavela mauyo, kwa icho wadalowa mkati ndi kumkambila Paulo. 17Paulo wadamtana mmoi wa asirikali ndi kumkambila, "mtenge mnyamatayu mpeleke kwa wamkulu wa asirikali wali ni mau wafuna kumkambila."18Msirikal yuja wadamtenga mnyamata ndi kumpela kwa wamkulu wa asirikali ndi kumkambila, PAulo yuja wamangidwa wadanitana ndi kunikambila nimpeleke mnyamatayu kwa iwe wali ndi mau ya kukukambila. 19Yuja wamkulu wadamgwila pajanja ndi kupita nae pamphepete, ndi kumfuncha, chinthu chanji ufuna kunikambila?''20Mnyamata yuja wadakamba, Ayuda avana kukupempha, ujenayo Paulo mawa pa baraza ngati afuna kujiwa nkhani zake. 21Kwa icho iwe uadavomela ndande wanthu makumi yanai, ajiikila chileso kuti saadya ndi saamwa mbaka ampe Paulo, chipano andolindila lamulo kuchoka kwa iwe.''22Yuja wamkulu wa asirikali wadamsiya mnyamata ndi kumkambila siwadamkambila munthu wali yonche kuti wanikambila nkhani ii. 23Waatana asirikali awili ndi kuakambila ikani asirikali okwela bulu ndi ali ndi nthungo simchoke zamu ya katatu usiku. 24Ikhani viyama wadakwele Paulo, mufikiche bwino kwa Feliki wamkulu wa chigao.25Wadalemba karata kwa mtundu uu. 26Klaudio Lisia kwa wamkulu wa chigao Feliki, moni. 27Munthuyu wadagwilidwa ndi Ayuda adali pafupi kumpa nde nidapita pamoji ndi asirikali nidampulumucha, yapo nidavela kuti iye ndi Mroma.28Nidafuna kujiwa ndande chiyani amuimba mlandu, kwa icho nidampeleka kubaraza. 29Nidaona kuti wadaimbidwa mlandu chifukwa cha mafuncho ya matauko yao, ndi siwaadaimbidwe mlandu ndi mau lililonche lienela kupedwa kapena kumangidwa. 30Kenaka idajiwika kuti kudali chisisi chimafuno kuchitika kwa iyeyo, mwa msanga nidamtuma kwanu. Nidaakamba yao amuimba mlandu apeleke mlandu wake pamaso panu, adalailana.''31Anyiwaja asirikali adavomela lamulo, adamtenga Paulo ndi kumpeleka ku Antipatri usiku. 32Siku lidachatila, asiriki ambili adaasiya okwela bulu apite pamoji ndi iye, anyiiwo adabwela. 33Ndi okwela bulu yapoadafika ku Kaisaria, ndikumpacha wamkulu wa chigao karata ija, adamuika Paulo pamaso pake.34Wamkulu wa chigao yapo wadaisoma karata, wadamfuncha Paulo wadachokela chigao chiti, yapo wadajiwa kuti ni munthu wa Kukilikia. 35Wadakamba sinikuvele iwe yapo saaje anyiawo akuimba mlandu, wadalamula waikidwe mnyumba ya chigao ya Herode.

Chapter 24

1Pambuyo pa masiku yasano, Anania kuhani wamkulu, wina wake wa Okota ndi akamba mmojhi wataniwa Tertulo, adapita pajha. Wanthu yawa apeleka milandu pakati pa Paulo. 2Paulo yapowadima pachogolo pa gavana, Tertulo wadayamba kumuimba milandu ndi kukamba kwa gavana, "kwa chifuko chako tili ndi mtendele waukulu, ndi kupenya kwako kuapeleka kung'anamuka kwa bwino pakati pa jhiko lathu, 3Basi kwa kuyamikila konche tilandila kila chinthu icho uchichita, kwamoni olemekezeka Feliki.4Nampho sinidakulemecha kupunda nikupempha univechele mau yochepa kwa. 5Kwa mate tampata munthu uyu wandeo, ndi wachiticha Ayahudi onche kupanduka pajhiko. Tena ni ochogoza madhehebu ya anazorayo. (penyelela mau ya mzele uu 24:6 6Ndi tena wadaesa kulithila hekal azi chimwechotidamgwila; palibemo mnakala za bwino za kale). (Penyelela mzele uu7Lisiasi, afisa, wadaja ndi kumtenga kwa mphavu mmanja mwathu, palibema mnakala za bwino za malembo ya kale.) 8Ukamfuncha Paulo kukhuza vinthu ivi, ata siukhoze ujhiyaluza ni chinthu chajhi tamuweluzila. 9Ayahudi nao adamuweluza Paulo, naakamba kuti ivi vinthu vidali va zene.10Liwali wadamkwezela jhanja kuti Paulo wakambe, Paulo wadayankha, "nijhiwa kuti kwa vyaka va mbili uli olamula wa jhiko lino, ndi nili ndi chisangalalo kujhikambilila namwene kwako." 11Ukhoza kuhakilisha kuti sizidafike masiku kupitilila maiku kumi ndi ziwili kuyambila yapo nidakwela kupita kumtamanda Kuyerusalemu. 12Ndi yapo adanipeza pahekalu, sinidachuchane ndi mnthu waliyonche, ndi sinidachite ndeo pakati pa msonkhano, wala pamasinagogi wala mkati mwa mujhi. 13Ndi wala sakhoza kuhakikisha kwako maweluzo yayoyaweluza pakati panga.14Nampho nivomela ili kwako, yakuti kwa njila nimtumikila Mulungu wa achaatate wathu. Ine ndi okhulupilila kwa yaliyonche yali mthauko ndin malembo ya olosa. 15Nili ndi ujasili umweujha kwa Mulungu uoata anyiwajha nao uo aulindilila, kujha kwa kuhyuka kwa akufa, kwa onche wene haki ndi opande haki. 16Ndi kwa ili nichita nchito kuti nikhale ndi dhamira ilibe hatia pamaso pa Mulungu ndi pamaso pa wanthu kupitila vinthu vonche.17Chipano pamalo pa vyaka vambili najha kupeleka mthandizo kwa jhiko langa ndi mphaso ya ndalama. 18Yapo nidachita chimwechi, Ayahudi akuti a Kuasia adanikomana mkati mwa chisngalalo chochukidwa mkati mwa hekalu, popande gulu la wanthu wala chipwilikiti. 19Wanthu yawa yao ifuika kukhalapo pachogolo pako chipano ndi akambe chijha alinacho pakati panga ngati ali ndi mau lalilonche.20Kapena wanthu yawa achinawene akambe kulakwa kwanji uo akuona kwanga yaponidaima pachogo pa bwalo la Kiyahudi. 21Ingakale kwa chinthu chimojhi ichonachikamba kwa mau yaponidaima pakatikati ao, ni kwa chifuko cha kuhyuka kwa akufa anyiimwe, "munilamula"22Feliki wadapachidw nkhani bwino kukhuza njila ndi wadaubwezecha msonkhano.wadakamba ''lisia jemedali yapo siwajhe panchi kuchokela Yerusalemu sinichoche lamulo pakati pa maweluzo yanu''. 23Ndeyapo wadalamula akida wampenyelele paulo nampho wakhale ndi siwadakhalapo munthu wa kwaaniza mabwenji yake asadamthangatila wala kumuendela.24Pambuyo pa siku za kutifeliki wadabwela ndi drusila mkazake uyo wadali muyahudi adatuma kumtana paulo ndi kuvechela kuchoka kwa iye nkhani za chikhulupi mkati mwa kristo yesu. 25Nampo Paulo yapowama kukambilana nae khuza haki, kukhala ndi kiasi ndi lamulo ilo silihe, feliki wadapata mantha wadayankha, pita kwakutali kwa chipano, nampho nikapaata nyengoncho, sinikutane."26Nyengo imueyo, wadakhulupalila kti paulo siwampache ndalama kwa chimwecho wadamtana mala kambili wadakambana nae. 27Nampho vyaka viwili yapo vidatha, prokio festo wadali liwali pamalopa feliki, nampho faliki wadafuna kujhisendeza kwa ayahudi, chimwecho wadamsiya paulo panchi pa kupenyeleledwa.

Chapter 25

1Ndiyapo festo yapowadalowa katika hekalu lijha ndi phambuyo pasiku zitatu wadapita kuchoka kaisalia hadi kuyerusalemu. 2Kuhani wamkulu ndi wayahudi mashuhuli adapeleka lawama dhidi yapaulo kulafesto ndi adakhamba kwa mphavu kwa festo. 3Ndi adamphempha festo fadhili pamwamba pa nkhani zapaulo wapheze kumtana kuyelusalemu iliakoze kumpha mnjila.4Nampho Festo wadayankha kuti Paulo wadali omangidwa kaika Kaisali, ndi kuti iye mwene siwabwele kumene chisangu. 5Wadakamba, "kwachimwecho, anjiwajha ambao akhoza kupita kumene ndi ife, ngati kuli chintu choipa kwa muntu uyu, mfunika umshitaki."6Pambayo pokala siku nane au kumi zaidi,wadabwela kukaisalia ndi siku lidachatha wadakhala phamphando wa kulamulidwa ndi kumlamula paulo wapelekedwe kwoke. 7Yapoadafika Wayahudi kuchoka Kuyerusalemu adaima pafuphi, adachocha malalamiko yambili yolemela amayo siadakoze kuyahakikisha. 8Paulo wadajitetea ndi kukamba, sizidi la jina la Wayahudi, si pamwamba pahekalu, ndi si pamwamba pa Kaisari, nachita voipha.'9Nampho Festo wamafuna kujipendekeza ka Wayahudi, ndi chimwecho wadayanka Paulo kwakukamba, bwa ufuna kupita Kuyerusalemu ndi kuhukumidwa ndi ine kupitila vintu ihi kumeneko? 10Paulo wadakamba, niima pachogolo pamphando wa lamulo la Kaisali ambapo nifunika kuhukumidwa. Sindidawalakwile Wayahudi, ngatiiwe umoujiwila bwino.11Ikakala nalakulila ndi ngati nachita ichochifunika nyifa, sinikana kufa nampho ngati lawama zao sikantu, palibe muntu wako za kunikabizi kwao, nimpempha kaisari." 12Baada ya Festo kukamba ndi baraza wadayanka," umpepha kaisari, udapite kwa kaisari.''13Baada ya siku zingapu, Mflume Agripa ndi Bernike adafika kaisari kuchita ziara lasmi kwa Festo. 14Baada ya kukala pamepo kwa ntauli yambili, Festo wadapeleka milaundu ya paulo kwa mflume wadakamba, muntu mmoji wadasidwa pano ndi Feliki ngati omangidwa. 15Yaponidali kuyerusalemu makuhani waakuluakulu ndi wazee wa Wayahudi adapeleka malalamiko pakati pa muntu uyu kwanga' nao adafucha pakati pa hukumu zidi yake. 16Kwaili ine nida yanka kuti si desturi ya roma kumchocha muntu kwa upendeleo badala yake, ohukumidwa ifunika kukala ndi nafasi ya kuwakabili oshitakidwa wake ndi kujitetea kupitila tuhuma zimene.17Kwachimuecho, Yapoadaja pamoji pano, sinidakoze kulindilila, nampho siku lidachata nidaka papando pahukumu ndi kulamula muntu uyu wapelekedwe mkati. 18Nyendo oshitaki yapoadaima ndi kumstaki, nidaganizila kuti palibe mashtaka yayakuluyayo yapelekedwa zidi yake. 19Pambuyo pake, adali ndi mabishano fulani amoji nae kuhusu dini yao ndi kuhusu Yesu ambaye wadali wafa, nampho Paulo wadai kuti wamoyo. 20Nidali namangidwa jinsi ya kupenya sala ili, ndi nidamfucha ngati walakapita Kuyerusalemu kuhukumidwa kuhusu vintu hivi.22Nampho Paulo yapowadatanidwa waikidwe chini ya ulizi kwa chifuko cha maamuzi ya mflume, nidalamula waikidwe mpaka yaposinimpeleke kwa kaisari. 21Agripa wadakambana ndi Festo ,"nikadakonda kumvechela muntu uyu."Festo wadakamba,"mawa siumve chele.''23Chimuecho mawa lake. Agripa ndi Bernike adafika ndi sherehe yambili, adafika kuukumbi ndi mafuru akijeshi, ndi mafuru akijeshi, ndi wantu mashuhuri ajiko, ndi Festo yapowadachocha maramulo, Paulo wadapelekedwa kwao. 24Festo wadakamba," mfulme Agripa, ndi wantu onche ambao mlipo pano pamoji nafe, mumuona muntu uyyu, jumuiya yonche yawayahudi kumene kuyerusalemu ndipano afuma nashauri , ndi nao adatimba kelele kwanga kuti siwadaishi.25Ndidaonaona kuti siwadachite chalichonche listahili nyifa, nampho kwa chifuko amtana mfulme, nidalamula kumpeleka kwake. 26Nampho nilibe chintu chamate cha kulemba kwa mfulme, kwa chifuko ii, nampeleka kwake, hasa kwako iwe. Mfulme Agripa, ili nipeze kukala ndi chintu cha kulembe kuhusu milandu. 27Pakuti ndiona ilibe mate kumpeleka omangindwa ndi bila kulangiza mashitaka yayoyamfuna.

Chapter 26

1Basi Angripa wadamkambila Paulo upachidwa kunjika mbilila ndo Paulo wadanyoshe janja lake kunjikambilila chimwe. 2Najiona nilini kukondwa mfumu Agripa dala kuchila mlandu wanga pachogolo pako lelo zidi ya malakamo yonchhe ya Wayahudi. 3Hasa kwa ndondi iwe onjwa wa ukalo wa Wayaudini mayunchho chimwechi nipempha umvechele.4Zene Ayahudi onchhe ajiwa umo na lamila tangu unyamata wanga katika jiko langa kuja Kuyerusalemu. 5Amjewa tangia kumayambo ni mfunika kuvomela kuti mikala ngati Mfarisayo, kanisa ni msimama waukulu kudini yatu.6Chapano naima nilamulidwe kwa ndamole ine nidapenya pangano ambalo mlungu wadachita wa achatawatu. 7Ili ni pangano ambalo mafuko yatu kumi na mbili ya kupalila uulandila ngati yamgwadile Mulungu kwa kujituma usiku ni usoma.Ni kwa ajili ya kulupalilo ili, Mfumu Agripa, kuti Ayahudi amimba mlandu. 8Kwa ndonde chiani walionehhe waganizila ni lodabicha kuti Mulungu wamyhusha wafa?9Nthawi imoji mdaganizila na mwene kuti mdakachita mambo ya mbili zidi ya jina mpulumusi wa Nazareti. 10Nidachita yaya katika Yerusalemu Nidamonga okulupalila ambili mndende ni nidali ni malamulo kuchoka kwa wakulu akulu anchembe kuchila chimwecho ni nthawi amapedwa nidabula chidindo zidi yao. 11Mara za mbili nidabula katika umo apemphela monchile ni nidaesa kwa chita akane chikulupi chao. Nidali ni hasira kupunda pamwamba pao ni nidatopola ata katika miji ya kuchilendo.12Nthawi yapo mimachila yaya,midapita kudameski,nikakala ni malumulo nikakala nimalumulo nimalangizo kuchoka kwa wakulu amehhembe; 13Yapo nidali mnjila nthawi ya usana,mfumu,nidaona domgalile kuchoka kumwamba lidali likalikuliko jua ni lidawala uuzungulila ine ni wamthu anyiyao amasafiri pamoji ni ine. 14Ife taonchhe yapo tidagwa ponchhi, midavela sauti imaliamba ni ine imakamba kwa mkambo wa kiebramia 'sauli, sauli! ndande chiami unizunja? nikulimba kwa iwe kuubula teki mchokoo.15Nde yapo nidakomnba"Iwe ni yami; Ambuye? Ambuye adayankho, ine ni Mpulumusi iye unizunja. 16Chapano inuka uime kwa myendo yako; ndonde kwa dala ili ine naonekana kwa iwe, nakusankhe ukale otumina ni mboni juu ya vichito ivo ujiwa kuhusu ine chapomo ni vichito nikulangize pambuyo. 17Ni nikuombole kuchoka kwa wamthu ni wamthu anaakamu yapo nikutuma. 18Kuchakula maso yao ni kwa choche kumdime kupita kuli domgalile kuchoka kuli nkhongono za satano amngomamukile Mulungu; daila apate kulandila kuchoka kwa Mulungu lekelelo la chimo ni chositidwa icho mwapachidwa anywaja adachochedwa kwa chikulupi chili liwonga.19Kwa icho, mfumu.Agripa, sinidakoze kulakwa maganizo ya kumwamba. 20Nampo, kwa amyiyao ali Kudameski poyomba, ni tena Kuyerusalemu ni jiko lonche la yudea, ni pia kuli wamthu amaiko ina, nidalalikila kutialape ni kumng'omamukila Mulungu, achite vichito vikozekome kulapa. 21Kwa ndande imeneyo Wayahudi adanigwila mkamisa adaesa kunipa.22Mulungu wadanitongatila mpaka saino, chimweshi niima ni uzene kwa wamthu akawaida ni kwa anyiwaja wakulu juu ya yaja ambayo openya patali ni Musa adakomba yachokele ni osati vino. 23Kuti Mpulumusi lazima wazunjindwe ni siwakale oyamba kuhyushindwa kuchoka kwa akufa ni kutangazila dangalila kwa Wayahudi ni wamthu amaiko.24Paulo wadamaliza kujikambilila, Festo wadakambakwa sauti yaikulu ; Paulo, iwe ni opambwane! Mayaluzo yako yakuchita ukale opombwane. 25Nampho wadakomba, ineosali opambwane olemekezedwa Festo nampho kwa kuji kulupalila ni komba mauya uzene okaoka. 26Pakuti mfumu wajiwe kuhusu vichilo hivi ni chimwecho ni Komba kwa uwazi wake kwa maana mlimi uhakika kuti paliji lalitonehhe labisidwa kwa iye;pakuti ili lidaitidwe pamphepete.27je ukulupalile openya paehogolo mfumu agripa mjiwa kuti ukulupalila. 28Agripa wadamkambila Paulo kwa nthawi pa itupi ukofa kumguzoine mkumchita okulupalila? 29Paulo wadakamba "nimpemphe Mulungu kuti kwa nthawi pa itupi au yaifali asatiiwepe bali kuti onchhe anivela lelo akalengatiine nampho poponda minyororo ya kundende."30Ndipo mfumu wadaima ni liwali ni Bernike nae ni anyiwaja adali akala pamoji ni anyiio 31Yapoadachoka kochezela adakambilo anyiio ni kukamba munthu uyu siifunika nyifa wala kumongidwa 32Agripa wadamkambila Festo ''munthu uyu wadakakoza kukala osililidwa ngati siwadakadula kupita mehogolo kwa Kaisari.''

Chapter 27

1Yapo idalamulidwa kuti tufunikana kusafiri kwa maji kupita Kuitalia adamkabidhi Paulo ndi amangidwa winancho kwa afisa mmoji wa jeshi la Kiroma uyowadatanidwa Julio, akikasi cha Agustani. 2Tudakwela meli kuchoka Kuadramitamu, iyo imasafiri mphepete mwa Asia. Mchimwecho tudalewa mnyanja Aristaka kuchoka Kuthesolanike ya Makedania wadapita pamaji nafe.3Siku idachotela tudatila nanga pakati pa muji wa Sidoni, yapo Julio wadamchitila Paulo kwa kumlandila ndi wadamruhusu kupita kwa achabwenji wake kulandila chikondi chake. 4Kuchoka pamenepo tudapita kunyanja tudasafiri kuzungurila kisiwa cha Kipro icho chidakinga mphepo, chifukwa mphepo imato tusumbua. 5Baada ya kusafiri pakati pamaji yalikalibu ndikilikia ndi Pamfilia ,tudaja kumira, muji wa Lisia. 6Paja yuja afisa wa jeshi la Kiroma, wadaipela moli kuchoka Kualexandria iyo imasafirikupita Kuitalia wadatukwela mkati mwake.7Baada ya kusafiri pang'onapang'ono kwa siku za mbili ndi badaye tudafika kwa taabu karibu ndi Kinidasi, mphepo siidalolezencho kuelekea njila imeneyo, mchimwecho tudasafiri mphepete mwa mtunchi wa Krete ndi tu kinga mphepo, mkabala ndi Salmone. 8Tudasafiri mphepeto mwa nyanja kwa ugumu, mpaka tudafika pamalo patanidwa Fari Haveni iyo ili karibu ndi mji wa Lasi.9Tudatenga nthawi ya mbili sana, ndi nthawi ya kumanga kwa Wayahudi adapitancho ndi chipana idali ndi hatari kuendelea kusafiri mchimwecha Paulo wadatuonya. 10Ndi kukamba , ''wachimuna, ndiona safari ambaya tu tuitenge siikale ndi madhara ndi asara yambili asatipe ya mizigo ila ndi chombo nampho ndi umoyo watu". 11Nampho afisa wa jeshi la Kiroma wadamvechela zaidi mbuye wake ndi olamula wa chombo kuliko vinthu vija ambavo vidakambidwa ndi Paulo.12Kwa chifukwa dooka sidakale pamalo pa rahisi kukala nyongo ya kuzizila ogwila nchito msitima ambili adashauri tusafiri kuchoka paja, ili kwa namna yaliyonche tukakoza kufika muji wa Foinike, tukale paja nyengo ya kuzizila, Foinike ndi dooke kumeneka Kukrete, ndi ipenya Kaskazini Mashariki ndi Kusini Mashariki. 13Mphepo ya Kusini yapoidayamba kuvuma pang'ono pang'ono, ogwila nchito msitima adaganizila apata chija amachifuuna adazula nanga ndi kusafiri mphepete mwa Krete karibu ndi.14Namphe baada ya nthawi ya ifupi mphepo ya mphavu, uwadatanidwa wa kaskazini mashariki, udayamba kutubula kuchoka chijala. 15Nyengo chembe yapochidalemeledwa ndi hali himeneyo, tudasafirishidwa ndiie. 16Tudatawa kupikila lija bendeka ilo limakinga mphepo ya bwani itanidwa kauda; ndi kwa taabu sana tudakeza kulamicha bwato.17Baada ya kuigula, adatumialuzi kuimanga chambe, adaepa kuti adakakeza kupita kumalo kwa mchenga wambili wa syiti, mchimwecha adachicha nanga ndi adaendechedwa pang'onapang'ona. 18Tudabulidwa kwa mphavu sana ndi mwela, mchimwela siku iyoidachotela ogwila nchi tamsitima adayamba kutaya mizigo kuchoka mchembe.19Siku ya katatu, ogwi la nchita msitima adayamba kuyachacha maji kwa manja yae achinawene. 20Nyengo yape jua ndi nthendwa sizida tuwalile kwa kwa siku zambili, bado mwela waukulu udatubula, ndi chikhulupi kuti tudakalamichidwa idacheka.21Baada ya kuti apita kwa nthawi ya itari bila chakudya, pamenepo Paulo wadaima pakati pao gwilanchito msitima wadakamba, "wachimuna idabidi mnivele, ndi sitidaka zula nanga kucheka Krete, ili kupata yaya madhara ndi hasara. 22Ndi chipano ndikupemphani mgwile mtima, kwa chifukwa sikukala ndi kutaika kwa umoge mkati mwanu, ingakale hasara ya chembepe.23Kwa chifukwa usiku uweudapita angale Amulungu, ambaye, mmeneyo mulunguine ndi wake ,ndi uyo ndi mgwadila angela wake wadaima mphepete panga. 24Ndi kukamba, "usaepa Paulo. Lazima uime pachogola pa Kaisari ndi ponya, Mulungu mkati mwa ubwina wake wakunikha anyizawa anche ambao asafiri pamaji nawe. 25Mchimwecho, wachimuna limbani mtima, kwa chifukwa ndimkhulupalila Mulungu, kuti siikale ngati umona kambidwila. 26Nampho lazima tupwetekedwe ka kubulidwa pakati pa baadhi ya madooko."27Yapo udafika usiku wa kumi na nne, yapatumandechewa kumeneke ndikumeneko ku nyanja ya Adratiki ngati usiku wa manane mchimwechi agwilanchita msitima adaganizila kuti akaribia pamtunda. 28Adatumia milio kupimila kunyoa kwa maji ndi adapata mita thelathini na sita, baada ya nyengo yayifupi adapi mancho adapata mita ishilini na saba. 29Adaapa huti tukoza kuganga myala, mchimwecho adachicha nanga zinai kuchoka pakati pa sehemu yeika nanga zinai kuchoka pakati pa sehemu yaika nanga ndi adapempha kuti umawa udakaja mapema.30Anyiwaja ongila nchita msitima amafu nafu na namna ya kuisia chambo ndi adazichicha mmaji zibwato zazing'onozing'ono za kulamichila umoyo, ndi adajichita kuti atayananga kuchoka pamalo papachogolo pa bwate. 31Nampho Paulo wadamkambila yaja asikari wa jeshi la Kiroma ndi anyiwaja asikari, "simkoza kulamicha ingakale anyiyawa wanthu abaki mchamba. 32Ndeyapo anyiwaja askari adadula vingwe va uja bwato ndi udasiidwa utengedwe ndi maji.33Nyengo dangalila a umawa yapelima chokela, Paulo wadaapimpha anche angalau adye kidogo, wadakamba,ii ndi siku ya kumi na nne mulindila bila kudya, simdadye chinthu. 34Mchimwecho ndi kupemphani mtenge cha kudya pang'ana, kwa chifu kwa ii ndi kwandande ya umeyo wanu,ndi palibe ata chichi limaji la mmutu mwanu uosiutaike. 35Yapo wadatokamba yameneyo, wadatenga mkate wadayamikila Mulungu pachogolo pamaso ya kila munthu, ndeyapo wadaumeze mkate wadayamba kudya.36Ndeyapo onche adagwila mtima ndi nao adatega chakudya. 37Tudali wanthu 276 mkati mwa chembe. 38Yapo adato kudya vakudya va kutosha, adachita chamba chiepuke kwa kutaya ngane mkati mwa nyanja.39Yapa idali usana siadajiwe pamtunda nampho adaona pamalo papamtunda ijapo padalewa mmaji iyoidali ndi mchenga wambili, adafotokezelana ngati akaza kuchiendecha chembe kuelekea pamenepo. 40Mchimwecho adazilegeza nanga adazisia mnyanja pakati pa nyengo imweyecha adalegeza vingwe za tanga ndi adainua malo ya pachogolo kuelekea kumphepo, mchimwecho adaelekea kumeneka kumalo kwa nchenga wambili. 41Nampho adaja pamalo ambapo myeeza iwili ya mmoji ipezana, ndi chamba chidaelekea kumchenga, ndilija malo la pachogolo pa chamba idakwama paja ndi siidakoze kuchoka nampho pamalo papa chegela pa chamba padayamba kuduka kwa chifukwa ya ukali wa mafunde.42Mpango wa anyiwanja asikari odali ndi kwaapa omangidwa ili kuti palibe ambayo wadaka sambilila ndi kuthawa. 43Nampho yujha askari wa jeshi la kiroma wadafuna kumlamicha Paulo mchimwecho wadauimika mpango wao, ndi wadalamula anyiwaja ambao akoza kusambilila, arumphe kuchoka mchamba huti ndia apite kumtunda. 44Ndeyapo wachimuna wina siachate, wina pamwamba pa vipande va vitambwa ndi wina pamwamba pa vinthu vinancho kuchoka kuchamba kwa njila ii idachokela kuti enche sitifike.

Chapter 28

1Yapo tidaikizidwa bwino tidajiwa kuti chilundwa Malta. 2Wanthu apajua osati kuti adatila ndika bwinope, ikapanda adasonkha moto ndikutanila taonche ndandi ya vula ndi kuzizila uko kudalipo.3Nampho Paulo yapo wadasonkhanicha mtoro wa nkhani ndikuikha pachoso njoka yaing'ono ya malovu yoipa wadatuluka mumtoto mujha ndandi ya kuunola, ndikujivilinga pajanjha lake. 4Waithu apajha yapo adaonanjokaijha indene kwa achinawene, munthu uyu ndi wakupha watawa kunyanja yamchele napho siwafunikukha wa moyo.''5Nampho uje nyoka ijha wadaiponyo pachoso ndisiwadapwetikedwe. 6Anyaio adamlindililia tuphi lake litupe kapina wagwe mwazizi ndikukumwalila. Nampho yapo amaphenya pa nyengo ya utali ndi kuona kuti palibe chinthu chadabwicha kwaiye adasintha maganizo yao ndi kunena kuti wadali Mulungu.7Pamalo paja pafupi padali nunda uo udali wamkulu wa chiumba munthu uyo wamatanidwa Pablio. Wadatilanila ndi kutisamala masiku yatatu. 8Idaoneka kuti atati wake a Pablio adagwilidwa ndi malungo ndi kupesa ndi Paulo wadapitila, wadaphimpha ndi kuwa akila manja ndi kuwalamicha. 9Baada ya lijha kutokea wandhu wina paja pachisiwani wajawadali wadwala pia wadapita ni kuwaponya. 10Wanthu adatilimkeza ulemu wambili. Yapo timajikonja kunyamuka adatipacha timavifuna.11Pambuyo pa miyezi itatu tidanyamuka pachombo, cha Iskanda iyo imapepheteledwa ndi kuziziia pa chilumbapo, ndi achogoleli wake adali mabali amawila. 12Pokafika kumujhi wa Sirakusa, tidakala pajha masiku ya tatu.13Kuchoka pajha tidanyamuka mbakana kukafika mujhi wa Regio, pambuyo pa masiku chimojhi mphempho ya kumwela inaonekana mwazizi, ndi pambuyo pamasiku yawili tidalowa mmujhi wa Putoli. 14Kumeneko tidaakomana mabale akumojhi ndi adatilanda kukula nao masiku ya sano ndi yawili. Njiia imweyo tidaika ku Rumi. 15Kuchoka kujha mabale anyiwajha, yapo adavela nkhani zatu, adajha kutilandi la kumsika wa Apias ndi nyumba za alendo zitatu. Yapo wadamuyamika Mulungu ndi kulimba mtima.16Yapo tidalowa Kuroma, Paulo wadaloledwa kukhala youha pamojhi ndi yiyha msikari wamamsunga. 17Idadi pambuyo pa masiku ya tatu Paulo wadaatana pamojhi anyiwaja wachimuna adali achogoleli pakati pa Ayaudi. Yapo adasonkhanika waadakambila, achabale pamojhi kuti sinididalalakwe chilichonche kwa muthu anjawa kapina kulakwila mwambo wa achambu yatu atichogolela, ndindachochedwa ngati mkaidi kuchokela Kuyerusalemu mbakana mmanja ya Aroma. 18Akate kundiuncha adakumbila kundimasula chifukwa padlije ndanda yofunika ine kuti ndi pendwe.19Nampho anyiwajha Ayahudi adakana, ndidakanamizidwa kuti mlandu wanga ndigwadile kwa Mfumu Kaisari ingakhale kuti sindimapeleko mlandu ku mtundu wanga. 20Ndande yogwadila mumu, ndikupemphani kuonani ndi kukamba namwe, ndande kuti Islael achiyekezela, ndamangidwa ndi chingwe ichi.21Adamkambila, "sitidalandilepo karata kuchokela Kuyuda yokukhuza iwe. 22Nampho tifuna kukuvela uganiza chiyani pakati pa gulu ili la wanthu yawa, chifukwa chake iwikana kwatu kuti tichuchana nao malo yaliyonche."23Yapo adapangana naye sikulu, wanthu ambili kupunda adaja yapo wamakhala wadaakambila ijha nkhani ndi kutilila umboni Ufumu wa Mulungu, wadayesa kwakokha kwa Yesu, kwa mtundu kawili kuchokela mmalamulo ya alosi kuyamba umawa mbakana ujhulo. 24Akumojhi adaguzika pakati pa mauya jha yamakambidwa, nyengo wina sadakulupalile.25Yapo adalepela kuvana achinawene kwa achinawene, adachoka pambuyo pa Paulo kukamba mau limoji Mzimu Oyera udakamba bwino kupitila Isaya mlosi wacha atate wanu. 26Wadakamba, pita kwa wanthu anyiyawa ukambe, mmakutu yanu simvele nanipho simvananavo, ndi kwa maso yano simuona nampho simjhiwa.27Ndande mitima ya wanthu anyiyawa yakala youma,makutu yao yavela kwa vutomaso yao atimila, kuti asajha kujiwa kwa maso yao, ndi kuvela mmakutu yao, ndi kuvana navo mmitima yao, ndi kung'ana mukancho, ndikuti ndidaka alamicha.''28Kwaicho mfunika kujiwa kuti Mulungu watumiza chipuluso chake kwa wanthu a mitundu, ndi savechele, (penyelela mzeleku. 29Nyengo wamakamba izi, Ayahudi adachoka, uku aliovutanavutana achinawene).30Paulo wadakala mnyumba yake yalendo panthawi ya viaka vuwili, ndi kulandila onche anyiyao adapita kwaiye. 31Wamalalikila ufumu wa mlungu ndi kuyaluza vinthu pakati pa yesu Kristo pa mphamivu zonche ndi padalije wadamchekeleza.

Romans

Chapter 1

1Paulo mtumiki wa Yesu Kristo, uyowadaitanidwa kukala mtume, ndikusangidwa pandande injili ya Mulungu. 2Iyi ndo ija injili iyo wadaihaidi kale kupitila alosi wake pakati pamalembo yoela. 3Ndi kuhusu mwanawake uyo wadabadwa kuchoka kolo la Daudi panjila ya tupi.4Iye wadatangazidwa pa mwana wa Mulungu kwa mbavu ya mzimu woyela poachidwa kwa kwa akufa Yesu Kristo atate watu. 5Kupitila iye talandila neema ndi utumiki kwa upole wa iani kati ya majiko yoje,pandande ya jina lake. 6Pakati pamaiko yaya, namwe piya matanidwa kukala Ayesu Kristo.7Utenga uu ndi kwaonje muli Kurumi, mukondedwa ndi Mulungu, mwaitanidwa kukala wandu oyela mtendele ndi ukale kwanu, ndi ufulu kuchoka kwa Mulungu atate watu ndi Ambuye Yesu Kristo.8Choyamba, nimuytamikile Mulungu wanga pakati pa Yesu pa ndande yanu onje, pandande ufumu wnu upembedwela pajiko lonje. 9Pakuti Mulungu ndi shaidi wanga, ambayo ndimtumikil kwa umoyo yanga pa injli ya mwana wake, paumo nilamila ndi kuwataja. 10Ndipo ndipemba pakuti pamapembelo yanga kuti panjila iliyonje nipeze potela ndikale ndikupeza chopano ndi chikondi cha Mulugu pakuja kwatu.11Ndiposo ndikumbila kuwaonani, ili ndipate kukunkhani anyiimwe pangono mtavu za mutima, ndipate kukulimbichani. 12Yani ndipenyelela kuitanidwa umoyo pamoji namwe panjila ya imani ya kila mmoji watu, wanu ndi kwanga.13Chopano abale, sinifuna mlepele kjiwa kuti, nyengo zambili ndapanga kuja kwanu, nambo nakanizidwa mbaka chopano nimafuna mchimwe ili kuti vipacho kwanu ngati ivojo muitima mwanu mwa wandu apajiko. 14Ndidaidwa nda Yunani ndi alendo pia, ojiwa ndi ajinga. 15Pachocho kwa upande wanga, ine ndi litayali kutangaza mau kwanu pia anyiimwe muli kumene kurema.16Pandande sindiionela soni pembel, pakuti ndi kukoza kwa Mulungu upeleka machiliso nkwa uyo wakulupilila kwa Muyahudi kwaza ndi kwa Muyunani piya. 17Pandande uzene wa Mulungu yaonekana kuchoka imani ata imani, ngati umoyalembedwa, "mwene ufulu si kale kwa imani."18Pakuti mkwiyo wa Mulungu yaonekana kuchoka kumwama kuposa kulakwa ndi kuononga kunje kwaa wandu, pakuti panjila yoipa ibisa uzene. 19Iyi ndi pandande, yonje yakoza kujuwikana pamwamba pa Mulungu ndi uzene kwao. Pakuti Mulungu wa kujiwichani.20Pakuti vindu vake ivo sivionekana bwino vili wazi choka kukonjedwa kwa njiko. Vieleweka kupitila vindu vidalengedwa vindu vimene ndi kukoza kwake kwa mtendele ndi asili yo lenga matokeo yake wandu alibe mpata. 21Iyi ndi pandande ingakale adamjiwa Mulngu sadamuyamike iye ngati Mulungu, ndipo sadampache mayamiko pambuyo pake avala vilekwa pa makhanizo yao ndi mitima yao yolakwa idatilidwa mdima.22Adajtuna kuti ndi ojiwa, nambo ali vilekwa. 23Aduusinda mtendele wa Mulungu uyo walibe kuwananga pa mfano wangope ya mundu wali ndi kuwananga ndiya mbalami ya vinyama ali ndi myendo inai ndi vindu vi kwawa.24Ndipo Mulungu adaasiya achate njanje za mitima yao kwa kuda, patupi pao ndi kunyozana pakati pao. 25Anyiiwo ausinda uzene wa Mulungu kukala mtila ndi anyiiwo amapemba ndi kutumkila vindu pambuyo pa otilenga ambaye waelekedwa muyaya. Amina.26Pandande iyi, Mulungu wadasiya ate njanje zao zafoni, pakuti a kazi wao adasinda utumiki wao obisa pachinja chidali kumbuyo ndi chisisi. 27Ndiposo wachimuna nao adasiya machitidwe yao ya chisisi pa akuti ndi kuikidwa ndi njanje dhidi yao achinawene anyiwawa adali wachimuna amachita ndi achimuna anjao yayo siyamalaize ndi adalandila mboto iyo sidali yoip kwao.28Pandande adakana kukala ndi Mulungu pazelu zao, adaasiya achate zelu zao izo sizimatandize achite vindu vao ivo sivimakuze.29Ajala ndi kuipidwa vonje, ndikuipa, njanje ndi kujipa ajala ndi janje, kupa, ndeo, kunyenga, ndi vichito voipa. 30Anyiiwonjo osengenya, onamiza, ndi oipidwa ndi Mulungu ali ndi ndeo, bwinya, ndi kujiona ndi okona voipa, ndi yao savela va yao wa bala. 31Anyiiwo alibe achijiwa yao sakulupilika, alibe chikondi ya mbadwa, di alibe lisungu.32Avana nazo njila za Mulungu, yecha kuti wandu achita voipa va njila imene afunika kupedw opandepe achita vindu yao achita vindu vo.

Chapter 2

1Kwaicho palibe pembelo iwe ulamula kwa mate pakati paya ja uyalamula uchita nkani zimwe zija. 2Nampo tijiwa kuti lamulo la Mulungu la uzene pakati pa wantu achita nkani ngati zimenezo.3Nampo iwe ganizila alala iwe ulamula wantu ngati izi ingakale nawencho wachita nkani ngati izi bwanji siulepele kupata lamulo la Mulungu? 4Kapena uganizila pang'ono kupunda pakati paukanyinji wa ubwino wake, uchedwa kwa lamulo lake, ndi kuvumilia kwake?5Ikapanda ume uli kalimbe kwa mtima wako ulije kulapa ujiikla wamwene kuikila ntawi ntawi umene ya kukwichidwa yani siku lija la kumasulidwa lamulo la bwino la Mulungu. 6Iye siwamlipile waliyenche chipimo sawasawa ndi vichito vake. 7Kwa anyiwaja kuwachazene wa vichito vao vabwino afunefune kukwezedwa ulemu ndiko sawanangika siwapanche ufuru osata.8Nampo anyiwaja ojifunilaoka, aliosachata uzene ikapanda avemeleza kuoneledwa kukwiichidwa ndi kukwiya ibwela. 9Mulungu sipeleka mavuto ndivato pamwamba pa malo tu pa muntu wachita voipa, kwa aAyahudi poyamba, ndi kwa Ayunanincho.10Nampo kukwezeka ulemu ndi mtendele sivije kwa waliyenche wachita vabwino kwa Muyahudi poyamba ndi kwa Muyunanincho. 11Chifuko kwa Mulungu kulibe upendeleo . 12Kwamate ngati muja ali ambili alakwila popande lamulo si ataike poande malamulo ndingati muja aliambili alakwila popande lamulo siataike popandemalamulo ndingati nmuja wena alakwila kwa tana ndi lamulo sialamulidwe kuchatana ndi lamulo.13Mate si aliosavenche lamulo ali ndi haki pachogolo la Mulungu ikapande anyiwaja achita lamulo siapachidwe veneleli. 14Chifuko chawantu ajiko alibe lamulo achita kwa mate nkani za lamulo anyio ali ndi lamulo kwa malo yao ingakale anyiimwe alibe lamulo,15Kwaichi alangiza kuti vichito vifuniks kes msfunikidwe ya lamulo yalembedwa mkati mwa mitima yao chofuna chao cha ochatila anyiiwo, ndi maganizo yao kapena vaamanga kapena kwapenyelela achinawene. 16ni sonincho kwa Mulungu yasiyachokele pakati pa ntawi imwne Mulungu siwachochokele malamulo ya vobisika va wantu vonche sawa sawa ndi injniri yaine, kwanjila ya Yesu Kristo.17Tikambe kuti ujutana wamwene Muyahudi, wakala palamulo sangalila kwa kujikweza pakati pa Mulungu. 18Uyajiwe mafunidwe yake ndi kuyayesa yamene siyalingana nayo pambuyo pakupachidwa ndi lamulo. 19Nde tikambe kuti wajipacha kulimba umwene wake nde ni chgoleli osapenya dangalila wa anyiwaja ali kumdima. 20Okonjelela osajiwa mpuzusu wa wana ndikuti ulinalo palamulo pamalo pa lamulo ndi uyaruzidwa kwa zene.21Iwe basi upeleka pamalo mwena bwanji siujiyaluza wamwene? Uwe ukambilla popanda kuba bwanji iwe ukuba? 22Iwe ukamba siumachita chigololo bwanji siuchita? Iwe vipidwa chintu chilije nkope, bwanji si ukuba mchalichi?23Iwe ujikweza pakati pamalamulo bwanji siumuika cha manyazi Mulungu pakati pakuukila malamulo? 24"Kwamate" jina la Mulungu lichodwa ulemu pakati pawantu ajiko chifuko chanu ngati umoya lembedwela.25Kwa mate kusuridwa kwa zenere kufunika ngati kuchata lamulo, nampo ngati iwe okama tauko kusurudwa kwako kukala ngati kosasuidwa. 26KWaicho ikakala kuti muntu siwadaswiidwe waendekela kugwira tauko bwanji ikakala siwada nswiide sikutengedwe langati wa lamulo? 27Ndiiye siwada swiidwe kwa mtundundu siwalamula ngati siwachatile lamulo!28Kwa mate iye osati Muyahudi wali kwa mate ya kubwalo atangati waswiidwa osati kuja kwa kubwalo nampo mkati mwa tupi. 29Nampo Iye Muyahudi wali mkati ndi kuswiidwa ndi kwa mtima pakati mwamtima oati mkati mwa malembo kukwezedwa kwa muntu kwa mtundu umeneo siuchokela kwa wantu ikaopanda ichokela kwa Mulungu.

Chapter 3

1Potela ndi ulemeleho utiwalinao Wayahudi? Ndi ulemelelo wa jando ndi chiyani? 2Ndi bwino kupunda kwa kila njila poyamba ya yonche, Wayahudi adapachidwa mavunukulidwe kuchokela kwa Mulungu.3Nampho si kale bwanji ikakala amojhi wa Wayahudi si adali ndi chikhulupi? Bwanji usakala ndi chikhulupi kwa anyiiwo sikuchite chikulupi cha Mulungu kukala chonamiza? 4Iyayi. Pambuyo pake, siya Mulungu waonekane kuti zene, ata ngati kila mundhu ni waunami, ngati umoidalembedwa, "Yakuti ukoze kuonekana kuti mwene malinga pa mau lako, ndi ukoze kukoza yapoulowa pa malamulo."5Nampho ikakala kuipa kwatu kulangiza malinga ya Mulungu, tikambe chiyani? Mulungu osati wakupa yapowachocha kuipila kwake, bwanji wali chimwecho? Nakambe kuchokelana ndi mate ya chimundhu. 6Po pande! Ndi mtundu uti basi Mulungu siwalilamule jhiko?7Nampho ikakala zene ya Mulungu kptila unami waine uchocha ukalo ka chifuko chake, kwa ndande chiyani nikati kulamulidwa ngati uyo wa machimo? 8Ndande chiyani tidanena, ngati umoatinamizila ndi ngati wena amoachimikizila kuti tinena, "tichite voipa, kuti yabwino yajhe''? Lamulo pamwamba pa anyiiwo ndi ya malinga.9Chiyani chipano besi? Tijhitetea takhinawefe? Iyayi kabisa. Pakuti ife tayari talamulila Wayahudi ndi Wayunani wonche pamojhi, yakuti alipanjhi pa machimo. 10Iyi ndi uumoyalembedwela: "palijhe uyo wachilungamo, ata mmojhi.11Palijhe mundhu uyo wazindila, palijhe mundhu uyo wamfunafuna Mulngu. 12Wonche agwa anyiiwo kwa pamojhi aliopande opande mate. Palijhe wachita yachilungamo, la, ata mmojhi.13Makolomilo yawo ndi kabuli ilo la masuna Lilimezawo zanyenga sumu ya nyoka ili panchi pa milomo yawo. 14Pakanwa pawo pajhala kuleswedwa ndi kupweteka. Myendo yawo ili kutamanga kumwaza mwazi.15Myendo yawo ili kutamanga kumwaza mwazi. 16Kuwananga ndi mavuto yali pa njila zawo. 17Wandhu anyiyawa siajhiwa njla ya mtendele. 18Palibe mantha ya Mulungu pachogolo pa maso yawo.''19Chipano tijhiwa kuti chalichonche tauko linena, linena ndi anyiwajha alipanchi pa tauko. Iyi ndi uti kila mlomo mmngidwe ndi chimwechon kuti jhiko lonche likoze kujhichocha kwa Mulungu. 20Iyi ndi kwachifuko palibe tupi siliwalengedwe malinga kwa vichito vya tauko pachogolo pa maso yake. Pakuti kupitila tauko ikijha kujhijhiwa kwa machimo.21Nampho chipano popande tauko, malinga ya Mulungu yajhiwikana. Wadachita umbani kwa tauko ndi olosa. 22Imeneyo ndi malinga ya Mulungu kupitila chikulupi pa Yesu Kristo kwa anyiwajha wonche anikulupalila kwa mate palibe mtundu wena.23Pakuti wonche achita machim ndi kuchepekedwa ndi ulemelelo lwa Mulungu. 24Awelengedwa Malinga chake kwa neema ya iye kwa njila ya chipulumuchi chidali pa Kristo Yesu.25Kwa mate Mulungu wadamchocha Kristo Yesu wakale chivanichano kwa njila ya chikulupi pa mwazi wake. Wadamchocha Kristo ngati umboni wa malinga yake, kwa dande ya kugisiya machimo yayo yapita. 26Pa uvumilivu wake yaya yonche yadachokela kuti kulingiza malinga yake nyengo ino ya chipano. Iyi idali kuti wakoze kuchimikiza mwene kukala malinga ndi kulangiza kuti wamuwelengela malinga mundhu walyenche kwa ndande ya chikulupi pa Yesu.27Kulikuti basi kujikweza? Kwa patulidwa kwa misingi iti? Misingi ya vochita? Iyayi, nampho kwa misingi yo kulupalila. 28Mmwemo timalizila kuti mundhu wawelengedwa malinga kwa chikulupi popande vichito va tauko.29Kapena Mulungu ndi Mulungu wa Wayahudi pe? Bwanji iye osati Mulungu wa wandhu w majhko nayo? Yetu, mayiko nayo. 30Ikakala kwa zene Mulungu ndi mmojhi siwawelengele malinga yawo aliwajanda kwa chikulupi, ndi osadulidwe jando kwa njila ya chikulupi.31Bwanji ife ting'anamula tauko kwa chikulupi? Iyayi, kumbuyo ya yameneyo, ife tichimikizila tauko.

Chapter 4

1Sitiambe chiyanincho kuti Abraham, tate watu kwa mtundu watupi, wapezake? 2Pakuti ikakala Abraham wadawelengedwa malinga kwa vichito, wadakakala ndi ndande yojielekela, nampho osati pamaso pa Mlungu. 3Nkha malembo yakamba bwanji? Abrahama wadamkulupilila Mulungu ndi idawelengedwa kti malinga.4Chapano kwa munthu uyo wachita nchito, malipilo yake siyawelengedwa kuti ndi lisungu nampho ngawa. 5Nampho kwa munthu uyo siwachita nchito nampho wamkulupilila iye wamuwelengela malinga munthu siakuzika Mulungu, chikulupi chake munthuyo chiwlendedwa malinga.6Daudi nae wakamba mdalso wa muntu mmene Mulungu wamwelengela malinga popande vichito. 7Wadakamba, adalisidwa amene voipa vao vakulunkidwa ndi machimo yao yavinikilidwa. 8Wadalisidwa munthu mmene ambuye samuwelengela machimo.9Bwa mdaliso uu uli kwa wanthu yao aumbalidwa kapena ndiyao osaumbalidwa. Pakuti tikamba kwa Abraham chikulupi chake chidawelengedwa ndi malinga. 10Kwa icho idawelengedwa bwanji? Nyengo Abraham watoumbvalidwa kapena wakali osaumbalidwe sidali nyengo yo umbalidwa nampho muosaumbalidwe.11Abraham wadalandil chizindikilo cha umbalidwa uu udali udindo wa malinga ya chikulupi wadatokala nacho wakali zochatila za chilangizi ichi wadachitidwa tate wa onche akulupalila, ingakale mateyake kuti malinga siiwelengedwe kao. 12Mate yake kuti Abraham wadachitika tate wa osati kwa anyiyao achoka na ndi ampho kwa anyiwaja achata mapozi ya tate wathu Abraham. Ichi nde chikulupi wadali nacho.13Mateyake silidali tauko kuti lidachochedwa kwa Abraham ndi kamu lake kuti saakale osiilidwa a jiko la panchi, ingakale, idali kupitila malinga ya chikulupi. 14Mateyake ngati anyiwaja atauko nde osiilidwa chikulupi chakalachaje ndi. 15Ndande tauko lipeleka kukwiya, nampho popande tauko kulibe kutauka.16Ndande iyi ichi chichokela mwa chikulupi kuti ikale kwa lisungu, zochatila zake ndi kwa kamu ionche ndi obalidwa wa osati yao ajiwa tauko, nampho na aniwaja achikulupi cha Abraham, mateyake iyende tate wathu taonche. 17Ngati umo yalembedwa, nakuchita iwe kukala tate wa maiko yambili, Abraham wadali munthu okulupalila Mulungu mmene wapacha akufa moyo ndi kutana vosakalepo kuti kuti vikalepo.18Kulekana ndi mitundu yonche ya kubwalo, Abraham wadalimbikila kukulupilila Mlungu mwa sikuzibwela, kwa icho wadakala tate wa maikon yambii ngati chija chidakambidwa nde umo siikalile kamu lako. 19Iye wadalije kuchepa mchikulupi. Abraham wadavomela kuti tupi lake mwene lidatokufa wadalindi vyaka vambili ndi kuti mkazi wake Sara wadali wa mbenda.20Abraham siwadaope ndande ya nkhani iyi nampho ndande ya chikulupi wadamkuzika Mlungu. 21Wadajiwa Mlungu siachite vonche ngati umo wakambila. 22Mateyake Mlungu wadamvomela kuti wadali munthu wa malinga.23Yapo ikambidwa wadamvomela siikambidwa ndande ya iye mwene yokape. 24Nkhani iyi itikuza ndi ife tikulupilila kuti Mlungu adaahyucha Ambuye Yesu kuchoka kwa wanthu akufa. 25Iye wadachochedwa wapedwe ndande ya machimo yatu, wadahyuka kuti tichitidwa wanthu a malinga.

Chapter 5

1Pakuti tawelendedwela haki kwa njila ya chikulupi, tili ndi mtendele wa Mulungu kwa njila ya Ambuye wathu Yesu Kristo. 2Kupitila ie ife tili ndi malo kwa njia ya chikhulupi pakati pa mwawi uu mkati mwake tiima, tisangalala pakati pa mphavu watipacha Mulungu kwa chifuko cha pambuyo, mphavu iyo sitigwilane nao pakati pa ufumu wa Mulungu.3Opande ilipe nampho pina tisangalala pakati pa mazunjo yathu, tijhiwa kuti mazunjo yabala kuembekeza. 4Kuembekeza kubala kuvomeleka, ndi kuvomeleka kubala mphavu kwa chifuko cha pambuyo. 5Mphavu ii siidulicha khumbilo, kwa chifuko chikondi cha Mulungu chataidwa pakati pa mitima yathu kupitila Mzimu Oyela, uyo wadachochedwa kwathu.6Kwa yapo tidali tikali odwala kwa nyengo yokwanila Kristo wadafa kwa ndande ya olakwa. 7Pakuti siikhale kulimba mmojhi kufa kwa ndande ya munthu mwene haki ii ni kuti ni kapena munthu wadakaesela kufa kwa ndande ya munthu wa bwino.8Nampho Mulungu wadvomeleza chikondi chake mwene kwahu, kwandande nyengo tidali tikali amachimo, Kristo wadafa kwa ndande yathu. 9Pothela kupunda kwa yonche, chapano pakuti tawelengedwela haki kwa mwazi wake, sitiomboledwe kwa chimwecho kuchokela pakati pa mpwai ya Mulungu.10Pakuti idalinyengo tidali oipa tidavanichidwa ndi Mulungu kwa njila ya nyifa ya mwana wake, pamalo pakuti tidatho vanichidwa, sitiomboledwe kwa maisha yake. 11Opande ivipe, nampho tisangalala pakati pa Mulungu kupitila Ambuye Yesu Kristo, kupitila iye chapano talandila kuvanichidwa uku.12Kwa chimwecho basi, ngati kupitila munthu mmojhi machimo yadalilowelela jhiko, kwa njila ii nyifa idalowelela kw njila ya machimo. Ndi nyifa idaenela kwa wanthu onche, kwa ndande onche adachita machimo. 13Pakuti hadi thauko, machimo yadali pajhiko, nampho machimo siyawelengeka nyengo palibe thauko.14Ata chmwecho, nyifa idatawala kuchokela Adamu hadi Musa, ata pamwamba pa yao sadachite machimo ngati kusavomela kwa Admu iye ni chifanizi cha uyowadakhaja. 15Nampho ata chimwecho, mphaso ya ulele osati ngati kulakwa pakuti idali kwa kulakwa kwa mmojhi ambili adafa, kupitilia kupunda mwawi wa Mulungu ndi mphaso kwa mwawi wa munthu mmojhi, Yesu Kristo, yapunda kuongezeka kwa ambili.16Pakuti mphaso osati ngati mayankho ya yujha wadachita machimo pakuti kwa madela yanjake, lamulo la adhabu idajha ndande ya kulakwa kwa munthu mmojhi. 17Kwa mate, idali kulakwa kwa mmojhi, nyifa idaenela kupitila mmojhi, kupunda anyiwajha yao sialandile mwawi wa mbili pamojhi ndi mphavu saatawale kupitila umoyo wa mmojhi, Yesu Kristo.18Chimwecho basi, ngati kupitila kulakwa kamojhi wanthu onche adali kukulamulidwa ata ngati kupitila kulakwa kamojhi kwa haki ya umoyo wa wanthu onche. 19Pakuti ngati kupitila kusavomela kwa munthu mmojhi ambili adachitidwa kuti amachimo, chimwecho kupitila kuvomela kwa mmojhi ambili sachitidwe wene haki.20Nampho thauko lidalowa kamojhi kuti kulakwa kukhoze kwenda. Nampho pamalon yapo machimo yodapunda kukhala yambili, mwawi udaongezeka mala kambili. 21Ii idachokela kuti, ngati machimo umoyadaenela pakati pa nyifa, chimwecho ata mwawi ukhoza kuenela kupitila haki kwa ndande ya umoyo wa muyaya kupitila Yesu Kristo Ambuye wathu.

Chapter 6

1Tikambe chiyani basi? Tiendelee kupitila dhambi ili chimwemwe chiongezeke? 2La ingakale. Ife tafa kuptila dhambi tikozancho kulomala kupitila chimwecho. 3Bwa simjiwa yakuti anyiwaja abatizidwa kupitila Kristo adabatizidwa kupitila mauti yake?4Tidali tazikidwa pamojhi naye kupitila ubatizo kupitila nyika, ichi chidachitika ili kuti ngati muja Kristo muja wadakwezedwela kuchoka mauti kupitila kuhyuka kwa Ambuye. Ili kuti ife tikoze kuenda kupitila upya wa maisha. 5Pakuti ikakala taunganishidwa pamoji nae katika mfano wa nyifa yake, sitiunganishidwe kupitila kuhyuka kwake.6Ife tijiwa kuti utu wantu wakale umalindililidwa pamoji nae, ili kuti tuphi la dhambi liwanagidwe ii idachokela ili kuti sitaendelea kukala atumwa adhambi. 7Iye wafa wachitidwa mwene haki kulingana ndi dhambi.8Nampho ngati thafa pamoji ndi Kristo, thi yamini kuti sitiame pamoji naye. 9Tijiwa kuti Kristo wahyuka kuchoka katika wafu, ndikuti osati mfuncho nyifa sichimtawalancho.10Pakuti ka khani ya nyifa ichowadafa kwa dhambi, wadafa mara kamoji kwa chifuko cho onche hata chimwecho.Maisha yayowaishi, waishi kwa chifuko cha Mulungu. 11Kwa njila imweyo, namwe pia mfunika kujiwelenga kukala wafu kupitila dhambi. Ila umoyo kwa Mulungu kupitila Kristo Yesu.12Kwa chifuko chimwenecho siudamramula dhambi ikutawele mthupi mwako ili kusudi ukhoze kuzitutamar zake. 13Usidachocha sehemu za thupi ako kupitila dhambi ngati vyombo vilibe haki, ila jichoche umwene kwa Mulungu, ngati anyiyaoali amoyo kuchoka kumautini ndi zichocheni sehemu za mathupi yanu ngati vyombo va haki kwa Mulungu. 14Msidalamula dhambi ikutawaleni, pakuti sitiliphanchi pa malamulo ila phanchi pa chisangalalo.15Chiyani basi? Tichite dhambi pakuti sitili phanchi pa malamulo napho phanchi pachiangalalo. 16Simjiwa kuti kwake iye ambaye mjichocha machinawene ngati atumiki ndiye ambaye namwe mkala atumiki wake, iye mfunika kumtii? Ii ni kweli hata ngati anyaimwe ni akapolo katika dhambi ambayo ipelekela mauti, au akapolo wa utii uoupelekea haki.17Nampho wayamikidwe Mulungu! Pakuti mdali akapolo adhambi, nampho mwatii kuchokela mmitima ya namna ya yaluzo yayo mdapachidwa. 18Mwachitidwa huru kuchokela kudhambi, ndi mwachitidwa akapolo wa haki.19Nikhamba ngati munthu kwa chifuko cha madhaifu ya mathupi yanu, kwa chifuko ngati mujha mdachochela viungo vanthupi yanu kuti akapolo kwa ukazuzu ndi uovu, kwa jinsi imene imene, chiphano chochani viungo va mthupi mwanu kuti akapolo wa haki kw utakaso. 20Pakuti yapomdali akapolo wa dhambi,m mdali huru kuali ndi haki. 21Kwa nyengo imeneyo, mdali ndi viphacho liti kwa ambaye kwa chiphano mupenya nchoni kwao? Pakuti mtokeo ya vinthu ivi nyifa.22Nampho oakuti chiphano mwachita huru kutali ndi dhambi ndi mwachitika akapolo kwa Mulungu, palibe chiphacho kwa chifuko cha utakaso: chichokela ni umoyo wa muyaya. 23Pakuti mshahara wa dhambi ndi mauti, ila phaso ya chajhe ya Mulungu ni umoyo wa muyaya kupitila Kristo Yesu Ambuye wathu.

Chapter 7

1Kuti simjiwa, achabale wanga (pakuti nikamba ni wanthu alijiwa lamulo), kuti lamulo limtawale munthu yapo wakala wamoyo?2Pakuti wamkazi wakwatiwa wamangidwa ni lamulo kwa yuja wammuna yapo wakala wa moyo, nampho ikakala wammuna wakafa, wakale wamasulidwa kuchoka lamulo la ukwati. 3Chimwecho basi, wakati wammuna wakali kuishi, ikakala waishi ni wammuna mwina watanidwe wachigololo. Nampho ikakala mmunake wafa, wamasulidwa kwa lamulo, ndikuti siwakala wachigololo ngati siwakale ni wammuna mwina.4Kwa icho, achabale wanga, anyiimwe pia mdaitidwa akufa kwa lamulo nkwa njila ya tupi la Mpulumusi. Yakala chimwechi dala mpate kulunjidwa ni mwina, kwa iye uyo wadayushidwa kuchoka ko akufa ili tukoze kumbalila Mulungu vipacho. 5Pakuti yapotidali hali ya tupi, kukumbila kwa machimo kudauchidwa katika viwalo vatu kwa njila ya lamulo ni kuibalila nyifa vipacho.6Nampho saino tamasulidwa kuchoka katika lamulo taifela ija hali imatupinga dala ife tipate kutumika katika hali ya mpya ya Mzimu, ni osati hali ya kale ya malembo.7Tikambenji basi?Lamulo ni chimo? Osati. Ata chimwechi sinidakajiwa chimo, sinidakala kwa njila ya lamulo pakuti sinidakalijiwa kukumbila ngati lamulo silidakakamba, "usakumbila." 8Nampho chimo idapata malo kwa lija lamulo ni idapeleka mkati mwanga kila mtundu okumbita pakuti chimo popanda lamulo yafa.9Nane nidaliwa moyo paja poyambita bila lamulo, nampho yapo lidaja lamulo, chimo idapata kukala ya moyo ndiine nidafa. 10Lija lamlo ambalo lidakapeleka kulama idang'anamuka kukala nyifa kwa ine.11Pakuti chimo idapata malo kwa lija lamulo ni idang'anamuka kukala nyifa kwa ine. 12Kwa icho tauko ni toela, n lamulo ni loela, la uzene ni la bwino.13Kwa icho basi lja lidali lidali la nyifa kwa ine? Sidakala chimwecho kabisa. Nampho machimo dala kuonekane machimo hasa kupitila ili ya bwino, idapeleka nyifa mkati mwanga ili lidali kuti pitila lija lamulo, machimo ikale yoipa kupunda. 14Pakuti tijiwa kuti lamulo chisisi chake ni cha muntima, nampho ine ni munthu wa tupi. nagulichidwa panchi pa ukapolo wa machimo.15Pakuti nichitalo, sinilijiwa bwino. Pakuti lija nilikonda kuchita, sinilichita, ni lija niliipala, nde ilo nilichita. 16Nampho ngati nilichita lija sinilikonda, nivomelezana ni lamulo kuti lamulo ni la bwino.17Nampho saino osatiine mtima wanga nilichita limenelo, bali ni lija chimo likala mkati mwanga. 18Pakuti mjiwa kuti mkati mwanga, yani mkati mwa tupi langa, Sichikala chinthu cha bwino. Pakuti kumbilo ya lili la bwino lili mkati mwanga, nampho simlichita.19Pakuti lija la bwino nilikonda sinilichita, bali lija loipa sinilikonda nde nichita. 20Basi ngati nichita lijasiilikonda, osati ine na mwene nilichita, bali ni lija chimo likala kati mwanga. 21Najiwa kuti kulichinthu mkati mwanga chnuifuna kuchita lili li la bwino, nampho loipa zene lili mkati mwanga.22Pakuti niliseketela lamulo la Mlungu kwa ulemu wa mkati. 23Nampho niona mtundu uliolekano katika viwalo va tupi langa. Vibula neo zidi ya ulemu wa chapano katika njelu zanga. Inichita ine ogwilidwa kwa ulemu wa chimo ili katika viwlo va tupi langa.24Ine ni munthu oandaula! Ni yani wanipulumuche ni tupi ili la kufa? 25Nampho mayamiko kwa Mulungu kwa Mpulumusi mbuye watu! Chimwecho basi. Ine namwene kwa njelu zanga nilitumikila lamulo la Mlungu. Ni kwa tupi iitumikila mtundu wa chimo.

Chapter 8

1Chipano basi palibe hukumu ya azabu pamwamba pao ali mkati mwa Kristo Yesu. 2Pakuti kanuni ya mtima wa umaya uja uli mkati mwa Kristo Yesu yanichita ine kukala humu patari ndi kanuni ya vochima ndi mauti.3Pakuti chija ambacho ramulo lidalepela kuchita chifukwa chidali chizaifu mkati mwa tupi, Mulungu wadachita, wadamtuma mwana wake kwa chifanizi cha tupi la chimawakale wanchembe ya chima, ndi wadahukumu vachimo mkati mwa tupi. 4Wadachita mchimwechi ili maagizo ya lamulo yakamilichidwe mkati mutu, ife ambao sitipita ko chota vinthu va mtupi, ila ka chota vinthu vinthu va mzimu. 5Anyiwaja achata tupi aganizila vinthu va mtupi, Nampho anyiaja achata mzimu aganizila vinthu va mzimu.6Pakuti ganizo la tupi ndi kufa, ila ganizo la mzimu ndi umoyo ndi chisangalala. 7Ii ndandelija ganizo la tupi ndi udani pamwamba pa Mulungu, pakuti siivomela lamulo la Mulungu, wala siikoza kuvomela. 8Anyiwaja achata tupi siakoza kumkwadilicha Mulungu.9Ata mchimwecho simuli mkati mwa tupi ila mkate mwa Mzimu, ngati ndi uzene kuti mzimu wa Mulungu uishi mkati mwanu. Nampho ngati munthu walibe mzimu wa Kristo, iye osati wake. 10Ngati Kristo wali mkati mwanu, tupi lafa kwa vinthu vochima, ila mzimu ulama kwa vinthu va malinga.11Ikakala mzimu wa yuja uyawamhyusha Yesu kuchoka kwa akufa waishi mkati mwanu, iye yuja wamhyusha Kristo kuchoka pakati pa akufa siwayaningencha matupi yanu ya kufa umaya kwa njila ya mzimu wake, waishi mkati mwanu.12Mchimwecho basi, achabalewanga, ife ndi adaidwa, nampho osati kwa tupi kuti tuishi kwa jinsi ya tupi. 13Pakati ikakala muishi kwa jinsi ya tupi, mli kalibu kufa. Nampho ikakala kwa mzimu musiya vichito cha mtupi, namwe simuishi.14Pakati ngati umo ambili aongozedwa ndi mzimu wa Mulungu, anyiywa ndi wana Amulungu. 15Pakati simdalandile mzimu wa mtumiki nchata muope. Badala yake, mdalandila mzimu wa kuchitidwa wana, iyo tulila, "Abba, yaninAtate!"16Mzimu uwo ulangizila pamoji ndi mizimu yatu kuti tuli wana Amulungu. 17Ikakala tuli wana, basi tuli osiidwilancha, kusiidwila ndi Mulungu, ndi ife tuliiosisdwila pamoji ndiKristo, Ikakala uzene tulaga ndi iye ili tupate kutukuzidwa pamoji ndi iye.18Pakutindi wolonga kwa nyengo ii kuti osati chinthu ndikalinganisha ndi ufulu uwosiuchakulidwe kwatu. 19Pakuti volibidwa vonche vipenyelela kwa khumbilo lambili kumasulidwa kwa wana Amulungu.20Pakuti malengedwe yadatimalidwa panchi pa mtima, popande kafuna kwake ila pandande yake iye wadavilemekeza panjila la tumaini. 21Kuti kuumba kwene nako sikuikide ufuru ndi kuchochedwa mkati mwautumiki wa kuwananga, ndi kulovyedwa pakati pa ufulu wa wana Amulungu. 22Pakuti tujiwa kuumba nakakudwala ndi kulaga kwa uchungu pamoji ata saino.23Osati mchimwechope, nampho ndi ife achinawefe tuli ndi ya Mzimu ife nafe kudwala mkati mwa mitima mwatu, nditulindilila kuchitidwa wana, yaani kulamichidwa kwa matupi yatu. 24Pakuti ndi kwa chifukwa ichi talamichidwa. Nampho chintu icho chidapenyeleledwa chikaonekana palbe kupenyeelancho, pakuti ndi yani wapenyelela chija chionekana. 25Pakuti tupenelela chinthu icho si tuchiana, tuchilindilila kwa hamu.26Kwa chifukwa chimwecho, Mzimu nao ututandiza pakati pa kulepela kwathu pakuti situjiwa kupempha umaifunikilana, nampho mzimu wene utupemphela kwa kudwala ukosikukozekana kukambidwa. 27Ndi iye waipenya mitima waijiwa njeru ya mzimu, ndande wapempha kwa niaba yao akulupalia kulingana ndi kukonda kwa Mulungu.28Nafe tijiwakuti kwa onche amkonda Mulungu, iye wachita vinthu vonche pamoji, kwa ubwino, kwaanyiwaja onche atanidwa kwa chifukwa chake. 29Ndande anyiwaja onche wadajiwa tangu mapema ndi wadasankhula tangu mapema alinganishidwe ndi chifanizi cha mwana wake ili iye wakale obaldwa oyamba mkati mwa achabale ambili. 30Ndi anyiwaja wadasankhula tangu mapema achameneo wadatanancha ndi anyiwaja wadatana, achameneo adawelenedwa malinga ndi anyiwaja wawelengela malinga, achameneoncho wadatukuza.31Tukambe chiyani basi pamwamba pa vinthu ivi? Mulungu wakakala bendeka latu, ndiyani wali pamwamba panthu? 32Iye uyosiwamsiilila mwana wake mwene. Nampho wadamchocha kwa chifukwa chatu ife onche siwakozebwanji kututandiza ndi vinthu vonche pamoji naje?33Ndiyani siwashitaki ochagulidwa Amulungu? Mulungu nde mene kuwawelengela malinga. 34Ndi yani siwahukumu adhabu? Kristo Yesu nde wadafa kwa chifukwa chatu, ndi zaidi ya yameneyo, iyencha wadamasulidwa. Naye watalwala pamoji ndi Mulungu pamalo pa ulemu,ndi iye watipemphela ife.35Ndi yani siwatichoche ndi chikondi cha Kristo? Dhiki, au shida, au kulaga au njala, au mariseche, au hatari, au chikwanj? 36Ngati umaidalembeledwa, "kwa faida zakotupedwa usana wonche, tudawelengedwa ngati mbelele yochinjidwa."37Pakati pa vinthu vimenevo ife tuli zaidi ya oshinda mkati waiye oyaatukonda. 38Pakuti atakunyengea kuti palibe kufa, wala umoyo, wala angelo, wala malamulo, walavinthu ivovilipo, wala vinthu vikuja, wala mphavu, 39wala yaliyo juu, wala yaliyo chini, wala kiumbe kinginecho chote, hakitaweza kututenga na upendo wa Mulungu, ambaye ni Kristo Yesu Bwana wetu.

Chapter 9

1Ndithu ndikunena uzenemkati mwa Kristo. Sindinena unami, maganizo yanga yakunditilila umboni pamoji mkati mwa Mzimu Oyera. 2Kuti kuli chisoni chachikulu ndimapwetekede yayakulu mkati mwa mtima wanga.3Ndikadakonda kuti ine namwene wake ndilesedwe ndi kuikidwa patali ndi Kristu ndande ya acha abale wanga. 4Anyaio ndi Aisraeli, achitika kukala wana, aulemelelo, achipanano, ndi mphoto ya malamulo, kulambila Mulungu ndi lonjezo. 5Anyaio ndi achogoleli kuti Kristo waja kwa ulemu kuvala thupi ili kuti iye de Mlungu wa vonche. Ndipowaelekeledwe muyaya. Amina.6Sikuti lonjezo la Mulungu lalepela kukwanila, nde kuti osathi munthu waliyonche wali Kuisraeli kuti Meisraeli wa zene. 7Ingakale vibadwa va Abrahamu kukala vibadwa vake vazene. "Nampho kupitila Isaka vibadwa vako vonche sivitanidwe."8Nde kuti wana athupi osati wana Amulungu. Nampho wana alonjezo apenyedwa kukala ngati vibadwa. 9Mateyake ili nde mau la lonjezo: "Pa nyengo iyi sindijhe ndi Sara siwapachidwa mwana."10Nampho osti ilipe, nampho pambuo pake Rebecca kupezela pa thupi kwa munthu mmojhi Isaka atate wathu. 11Kuti wana adali akali osabadwe ndi siwadachite choipa chalichonche kapena chabwino. Kuti ganizo la Mlungu kuchokana ndi chisankho li ime. Osati kwa vichito, nampho pa ndande ya yujha watana. 12Lida kambidwa kwa iye, wamkulu siwamtumikile wa mng'ono. 13Ngati umo yalembedwela: "Yakobo ndidamkonda nampho Essao ndidamwipila."14Nampho tikambe chiyani? Kuti kwa Mlungu kuli choipa? Noto. 15Pakuti wakamba kwa Musa, sindidakale olekelela kwa uyo sindimlekelele ndi sindidakale walisungu kwa uyo sindimlengele lisungu. 16Kwaicho osathi ndande iye wafuna, ndi osathi ndande iyo wathawa, nampho kwa ndande ya Mulungu, iye walangiza lisungu.17Pakuti malembo yakamba kwa Farao, pandande iyo ndidakukweza, kuti ndikulangize iwe mphamvu zanga, ndikuti jhina langa lilengezedwe mkati mwa maiko yonche. 18Kwaicho Mlungu wakhala ndi lisungu kwa waliyonche wamkonda, kwa iye wamkonda ndikumchita kukhala wa mbwinya.19Nde siunikhambile, ndande chiyani wakalikuona kulakwa? Yuti wadalimbikila kufuna kwake? 20Pambuyo pake munthu, iwe ndiyani uchuchana ndi Mlungu? Ikhozekana icho chapangidwa ndi Mlungu ndi doti, ndande chiyani wandichita chimwechi ine? 21Bwanji oumba wai ndi lamulo pakati pa dothi? Kukonja mbiya kwa kugwilila nchito kuchokela dothi limwelija? Ndi mbiya injake ndande ya kuchitila nchito masiku yonche?22Bwanji ngati Mulungu, wakalangiza kuipila kwake ndi kuchita mphamvu zake kujiwikana, wadalimbikila kupunda inthu va mphwayi vidalipo kuwananga? 23Bwanji ngati wadachita chimwechi kuti walangize kuchuluka kwa ulemelelo wake pa vinthu va lisungu, ivo wadata kuvipanga pa ndande ya ulemelelo? 24Bwanji ngati wadachita ata kwa ife wadatitana, osati kuchokela kwa Ayahudi, ampho kuchokela kwa wanthu ajhiko?25Ngati umo wakambila mkati mwa Hosea: "sinditane wanthu wanga anyiyao sadali wanthu wanthu wanga okondedwa wake iye uyo siwadakondedwe. 26Ndi silikale kuti paja lidakambidwa kwa anyiyao, anyaimwe osathi wanthu wanga! Pajha satanidwe wana Amlungu wa moyo."27Isaya walila pakati pa Israeli, ngati Aisraeli akadakhala ngati mchenga wa kunyanja ochepa nde anyiyao saomboledwe. 28Pakuti Ambuye satenge mau lao pa jhiko, chielaela pokwanicha. 29Ngati Isaya umowadakambila chiyambo ambuye amphamvu zonche siwadatisiile mmbuyo vibadwa vathu. Tiadakala ngati Sodoma ndi Gomora.30Sitikambenje? Kuti wanthu ajhiko adali osafunefune uzene, adapata uzene pa chikulupi. 31Nampho Israeli, wadafuna lamulo la zene, siwadalifikile.32Ndande chiyani osathi chimwecho? Ndande sadachathe chikhulupi, ikapanda pavochita adajikuwala pamwamba pa mwala wakujikuala. 33Ngati umo yalembedwela, penya ndagoneka mwala wakujikuala mkati mwa Sayuni ndi mwala olakwa, uyo siwakulupalile mkati mwa ili siwapata mwano.''

Chapter 10

1Abale, chofuna chamtima wanga ndi pembo langa Kwamulungu ndi pandande pulumusidwa kwao. 2Pakuti Pakuti ndikupenyani kuti mujituma pachifukwa cha Mulungu, nambo opande pandande yazelu. 3Pakuti sadajhiwe chofuna cha Mulungu , ndi afuna kumanga chofuna chao achinawene sadali ovela pa chofuna cha Mulungu.4Pakuti Kristo nde wakamiliza wa khan ya uzene pakila mundu wa vana navo. 5Pakuti Musa walemba kupiti uzene owo ubwela kuchokana ndi shaliya munda uyo wachina cha bwino cha shaliya siwakale pauzene uu.6Nambo uzene uwo suchakana ndi ni ufulu ikamba mchmwe, usidakamba mutima mwako, yani siwakwele kupita kumwamba? (Iyi ndi kupeleka Kristo pamoji). 7Ndi siudakamba, yani siwachike mjenje? (Iyi ndikumpeleka Kristo kumwamba kuchoka kwaakufa).8Nambo ikamba chiyani? Maulili pafupi ndiiwe, pa mau yako ndi pamtima pako limene ndimau la ufulu io tili kambilila. 9Pakuti kuti pakamwa pako uvomela Yesu yakuti ndi atate, ndi kuvomela mutima mwako kuti Mulunu wadamuuncha kuchoka kwa akufa si uokoledwe. 10Pakuti kwa mtima mundo wakuvandi kupata uzene, ndi kwa pakamwa wavomela ndi kuokoledwa.11Pakuti malembo yakamba, kila uyo wavananae siwapata njoni. 12Pakuti palibe chosiyana pakati pa Muyahudi ndi Muyunani, pakuti wa Ambuye ndi wawanja ndi Ambuye aonje, ndi wachuma kwa onje atana. 13Pakuti kula mundu uyo walitila jina la Mbuye siwaokoledwe.14Panjila yanji akoza kumtana iye uyo sama mlupalile? Ndi njila yanji aoka kuvana navo panjila yaka uyo sadamvele? Ndi savele bwanji ngati palibe wakwalikila? 15Ndi njisi yaji akoza kulalika ingakale atumidwa? Ngati umo yalembeledwa, "njila yanji ndiya bwino ywendo wajakambila khani zo kondwecha zavindu vabwino!"16Nambo oje sadavechele pembelo. Pakati Isaya wakamba, Ambuye, ndiyani wavela mau yatu? 17Ndipo kuelesedwa kukuja pambyo povela, ndikuvela pamavu la Kristo.18Nambo ndikamba bwa sadavele? Etu, pauzene sana "mau lao latochoka kubwalo pa jiko lonje, ndi maulao kupita kumatelo kwajiko."19Kuposa kwa voje, ndikamba, bwa izilaeli sadajiwe? Pakuti Musa wakamba, sinikuyambeni kukutilani janje kwa wandi opande ajiko. Pandande la jiko ilo savela, sinikuyambeni mbaka mkwiye.20Ndi Isaya mundu okulupililika sana ndi wakamba, midapezeka ndamjiwaja yao sadanifune, ndidaonekana kwayoo samanifune. 21Nambo kwa Iziraeli akamba, "sikuzojendida kweza manja yanja kwayao samanivele ndi kwawandu olimba."

Chapter 11

1Kwaicho nikamba bwanji Mulungu wadakawa achiwanthu wake? Ata pang'ono. Pakuti ine nanencho ndili Mwizraeli wafuko la Abrahamu, wa kamu la Benyamini. 2Mulungu siwaodekana achiwanthu wake, wadaajiwa chiyambilepo bwanji simujiwa malembo yanena bwanji pakati pa Eliya mmene wadampembeza Mulungu pakati pa Israeli? 3"Mulungu waapa orota wako, naoncho abomola walo ya mapempelo yako Ine ndeke ndekalila nanencho au funa umoyo wanga"4Nampo yauko la Mulungu likamba chiyani kwaiwe? Nasunga ndende yanga wantu elfu saba achaamene siampigira maombono baali. 5Ata chimwecho nyengo iinoyachopano alipo wena akalila chifuko chasankulidwe la mtendele.6Nampo ikakale kwa mwawi osatincho kwa vichito mene wake mwawi osatincho kwa vichito mwene wake mwawi siukalancho mwawi. 7Chiyanincho basi? Nkani imene Israeli wadalimkulifuna siwada chipate ikapanda osankulidwa adachipata ndiwena adapachidwa mpavu. 8Ndengati umoidalembedwa, "Mulungu waapacha mtima osatwa, maso dala side penya ndi makuti dala siadavecha mpaka lelo."9Nayenche Daudi wakamba, "siyameza zao zikale nkoka msampa, malo yojikonowala, ndikubwezela mbwezo pakati pao. 10Siya maso yao yatindwe mdima dala siada koza kupenya ukaokwalamicha misana yao ntawi yonche."11Mmwemo ndikamba, "Bwanji ajikono wale mpaka kugwa?" Siido kala chimwecho ntawi zonche pambuyo pake, pakulepela kwao kupurumuka wa bwella kwa wantu ajioko dala kuti achinawene wake akale ndi wivu. 12Chapano ikakala kulepela kwao nde kuwino kwajiko ndingati kulepelakwao nde kuwina kwajiko kiasi gani zaidi siikale kukala bwino kwao?13Ndi chapano ndi kamba ndi anyiimwe wantu ajiko lina, ndikurupalila nchito zanga. 14Kapena sindiatile mtima woipa al tupi limoji ndiine kapenasitiapurumuche ochepa wao.15Mate akakara kukanidwa kwao ni mavemelezano ndijiko, kulandichidwa kwao sikukale bwanji ikapanda umoyo wao kuchokela kwa wantu akufa? 16Ngati vipacho vo yamba ni kuikila ndi mmenemo ili pa muumbo wa ufa ngati mizo kuikila ntawi na zoncho mmwemo.17Nampho ngati vochepela ntawi zachulidwa ngati iwe ntawi za mizeituni yamtengo ude vyalidw pakati pao ndingati udeli pamoji nao pamiso ya kuwinayamiza itumi. 18Siutajitamila ntawi nampho ngati utamila siiwe uitandiza mizo ikapanda mizo ikutandizaiwe.19Mmwemo sikukambe, ntawi zidedulidwa dala kuti nipeze kuvyalila pajenje. 20Mmwemo zenendi chifuko chosa kurupalila kwao adadulidwa nampho iwe udaima gangang'a chifukwa cha chikulupalila chako siudajiganizila wamwene kwa mtundu wa pamwamba kupunda ikawe opa. 21Kwa mate ngati Mulungu siwadazisie ntawi za chilengedwe siwakusilila iwencho.22Penya basi vichito vabwino ndi kukalipa kwa Mulungu kwa malo yamoji kukalipa kudaja pamwamba pa Wayahudi acha amene adagwa nampo kwa pampete pena ubwino wa Mulungu ukuja pamwamba paiwe, ngati siukale pa ubwino wake.23Ndingaticho siandekela pakati pa sakukurupalila kwao si avyalidwencho mate Mulungu wali ndi kukozekana kuvyalancho. 24Kwa mate ngati anyiimwe mdandaulidwa kubwalo kwa umene kwa chilengedwe mizaituni ya ontengo ndi ikunyume cha chilengedwe mdavyalidwa pa mizaituni yabwino osati kupunda anyiwaja Ayahudi acheoneme aningati ntawi za chilengedwe?25Ndili ndi mate ache abale sindifuna simdajiwa kuchana ndi sirti dala kuti simdakala ndikuganiza pakati po ganizila kwanu mwachinawne siri ii kuti kulimba kwachokela pakati pa Israeli pakana katela kwa jiko yapo sikufikile.26Mmwemo Israeli yoncho siaporo muke, ngati umoyalembedwela: "Kuchokela Msayuni siwaje Mpulumsi siwauchoche kuipa konche kuchokela kwa Yakobo. 27Ndi ili silikale pangamo langa pamoji ndi anyiimwe ntawi yapo sindiyachocha machimo yao."28Kwa maloyena pakati pa injili siakaipile chifuko chano kwa malo yena chifuko cha sau kulola cha anuye Ambuye. 29Pakuti mpaso ndikutanidwa kwa Mulungu sikungana mule.30Pakuti mmayambo anyaimwe mdasimpana ndi Mulungu. Nampo chapano mwalandila Upulumuchi chifuko cha kufipana kwao. 31Kwanjila imeyo, chapano anyiyawa Ayahudi asanduka mateyake ndi kuti kuchokela ndi lisungu mwalilandile anyiimwe akozayancho kulandila Upulumusi. 32Mate Mulungu wa Amanga wantu wonchepakati povochite voipa delakuti wakoze kuwachita ubwino onche.33Mweneo ili kuvina ndi maganizo yabwino ndi pangizo lagwino la Mulungu, sizi chifidwila kafukufuku nmalamulo yake ndi njila zake siziiwike. 34Mate yani poyamba wadampacha chinthu Mulungu, dela walipaidwencho?35Kapena yani poyamba wadampacha chinthu Mulungu, dela walipaidwencho? 36Pakuti kuchokela kwaiye ndi kwanjila yake kwaiye vinthu vonche vilipo, kwaiye kukale uful osata. Amen.

Chapter 12

1Kwa icho nikupemphelani achabale kwa malisungu lao Mulungu, yachocheni matuphi yanu ikale nchembe iyo ili ya moyo, yoyela, iyoivomeleka kwa Mulungu imeneyo ndi ibada yanu yene mate. 2Wala msadauichatiza mtundu wa jhiko lino, ikapanda mng'anamulidwe kwa kuchitidwa achipano maganizo yanu, chitani chimwechi mpeze kjhiwa chikondi cha Mulungu chili cha bwino, cha kumkadwilicha ndi chokwanila,3Kwa mate ndinena, kwa ndande ya neema iyonapachidwa, kuti kila mundhu uyo wali mmojhi mwenu siwafunika kuganizila kupitilila pa mwamba pake niye mwene. Kusiyana imo inafunikila kuganizila kwa ulemu, ngati umo Mulungu wapacha kila mmojhi kiasi fulani cha chikulupi.4Pakuti tili ndi viwalo vonche vili ndi nchito imojhi. 5Mmwemo ncho ife tititaamili tili upi limojhi pa Kristo, ndi viwalo kila mmojhi kwa mnjake.6Tili ndi nchito zili zazopambana pambana kwa kadiri ya neema mwapachidwa. Ikakala nchito ya mundhu ni ulosi, nde ichitike kwa kadiri ya chikulupi chake. 7Ikakala nchito ya mundhu ndi kugwila nchito nde watumikile. Ikala nchito ya mundhu, ndi kuchocha, wachite chimwecho kwa kuchocha. 8Ikakala nchito ya mundhu ndi kutondoza mmwemo watondoze. Ikala nchito ya mundhu ndi kuchocha, wachite chimwecho kwa kuchocha. Ikakala nchito ya mundhu ndi kuchogoza, lichitike kwa kusamala. Ikakala nchito ya mundhu ndi kulangiza lisungu, lichitike kwa chimwemwe.9Chkondi sichidakala ndi kupa. Ipilani loyipa: Mgwililie yali ya bwino. 10Kukuza chikondi cha abale, kundanani anyiimwe kwa anyiimwe. Kukuza ulemu, limekazanani anyiimwe kwa anyiimwe.11Kukuza kulimbikila msadakala akugwa mtupi. Kukuza mzimu, mkale ndi shauku. Kukuza AMbuye, mtumikileni. 12Kondwani pa mphavu mlinazo kuuza pamasiku yabela. Mkati ndi kulindilila pa mavut yanu. Mlimbikila mwa kupemphela. 13Mgwilizane mwa yofunika ya mwaokulipila. Funani nila za mbili za kulangiza kuchocha.14Afunileni mwawi wonche akupwetakaani anyiimwe, mwapache mwawi ndi msalwesa. 15Kondwani pamojhi ndi anyawo akondwa, lilani pamojhi ndi anyiyawo alila. 16Mkale ndi maganizo ya mojhi anyiimwe kwa anyiimwe. Msadaganizila kwa dama, nampho avomeleni wandhu wa ntundu wa panchi. Msadakala ndi ulemu pamwamba pa maganizo yanu mwachinawene.17Msadalipa mundhu walyonche loyipa kwa loyipa. Chitani vichito vabwino pamaso pa wandhu wonche. 18Ngati ikozekana, ngati umoidaikidwa kwa anyiimwe, mkale ndi mtendele ndi wandhu wonche.19Okondedwa msadalipilila chisasi mwachinawene, nampho ipacheni malo mbwayi ya Mulungu. Kwa mate yalembedwa; "kulipizila ndi kwanga, ine sinilipe." wanena Ambuye. 20"Nampho ikakala oyipa waiwe wali ndi njala mdyeche, Wakakala ndi lujho, mmweche. Kwa mate ukachita chimwecho, siumpalile makala ya moto pa mwamba pa mutu wake." 21Usadalepela ndi choyipa ikapanda uoze choyipa kwa chabwino.

Chapter 13

1Kila munthu walemekeze matauko ya boma, kundande matauko yonche yachoka kwa Mulungu, ndi yao aimilila aikidwa ndi Mulungu. 2Uyo wakana matauko ya achogoleli wakana lamulo la Mulungu ndikuti yao achita chimwechi ajipelekela chilango achinawene.3Pakuti oimilila matauko saaofya wanthu ka vochita vabwino nampho kwa yao achita voipa, chipano ukafuna kuti siudamuopa wamatauko chita vabwino nae siwakuelekele. 4Pakuti ndi mtumiki wa Mulungu wachita nchito pa pindu lako, nampho ukachita voipa siufunike kumuopa, pakuti wakoza kukulanga iye mtumiki wa Mulungu, kualangiza kukwia kwake kwa anyiao achita voipa. 5Kwa icho ni tauko kualemekeza ali ndi malamulo osati ndande ya kukwia kwa Mulungu nampho ndande nde umo ifunikila.6Ndande imweyo msonkesha sonkho pakuti achogoleli amtumikila Mlungu kuti akwanilicha icho afunikila kuchita. 7Mpacheni kila mundhu malinga yake wafu sonko, sonkho, wafunika ulemu mpacheni ulemu.8Msakala ndi ngawa ndi mundhu walionche ingakale ngawa la kukondana, pakuti uyo wamkonda mnjake wakwanilicha tauko 9pakuti kukamba usadwita chigololo, usapa, usaba, usakumbila ndi ikakala po injake zonche zilimkati mwa iyi imoji kuti mkonde wa pafupi wake ngati umo ujikondla umwene, 10uyo wamkonda wapafupi wake siwangamchitile voipa kwa icho chikondi nde chikwanilicho cha tauko.11"tikajiwa nthawi youka mlitulo yato wandikila pakuti chipano chipulumuso chatu chili pafupi nafe osati ngati yapo tidayamba kukulupilila." 12Usiku wapitilila kupunda, usana wawandikila kwa icho tivule vichito va mdima ndi tivale zida za dangalila.13Usiku wapitilila kupunda, usana wawandikila kwa icho tivule vichito va mdima ndi tivale zida za dangalila. 14Kwa icho avaleni Ambuye Yesu, ndi msalipenya tupi, ndi kukweleza kumbilo lake.

Chapter 14

1Mlndileni waliyonche uyowali odwala pakati pa chikhulupi, popande kuchocha lamulo kukhuza maganizo yake. 2Munthu mmojhi wali ndi chikhulupi cha kudya chalichonche, mwina uyowali wangokudya ndio.3Munthu uyowakudya kila chinthu wasadamdelela uyosiwakudya kila chinthu. Ndi iye siwkudya kila chinthu siwadamlamula mwina uyowakudya kila chinthu pakuti Mulungu wathokumlamula. 4Iwe ndiyani, iwe uyoumlamla mtumiki uyowali chuma cha munthu mwina? Pamaso pa Ambuye wake kuti kuima kapena kugwa. Nampho siwaimichidwe, pakuti Ambuye akhoza kumchita kuti waime.5Munthu mmojhi wamlemekeza siku limojhi kuliko linjake. Mwina wamlemekeza kila siku sawasawa, ebu kila munthu wakumbilichidwe pakati pa njelu yake mwene. 6Iye uyowagwila siku, waigwila kwa ndande ya Ambuye. Ndi kwa iye wakdya, wudya kwa ndande ya Ambuye, pakut wampacha Mulungu mayamiko. Uyo siwakudya, wajimangila usadya kwa ndande ya Ambuye iye nae wachocha mayamiko kwa Mulungu.7Pakui palibe uyowalama kwa kujhiwa kwake. Ndi palibe uyo wakufa kwa ndande yake mwene. 8Pakuti ikakhala tilama, tilama kwa ndande ya Ambuye. Ndi ikakhala tikufa, tikufa ka ndande ya Ambuye. Basi ikakha tilama kapena tikufa tili chuma cha Ambuye. 9Pakuti ni kwa chikhulupi ichi Kristo wadafa ndi kulamancho. Kuti wakhale wa onche akufa ndi amoyo.10Nampho iwe, kwa chiyani umlamla m'bale wako? Ndi iwe kwa chiyani umdelela m'bale wako? Pakuti ife taonche sitiime pachogolo pa mpando wa malamulo wa Mulungu. 11Pakuti yalembedwa, "ngati umo nilamila," akamba Ambuye, "kwanga ine kila bombono siligwade, ndi kila lilime silichoche ubwino kwa Mulungu."12Chimwecho basi kila mmojhi wathu siwachoche vochita vake mwene kwa Mulungu. 13Kwa chimwecho, sitidaendekeancho kulamulana, nampho pambuyo pake lamula chimwe, palibe uyo siwaikechochekeleza kapena msampha kwa m'bale wake.14Nijhiwa ndi nakhumlichidwa pakati pa Ambuye Yesu kuti palibe chinthu icho chili njisi chene ndi kwaiyepe uyowaganiza kuti chalchoche ni najisi pakuti kwake ni najisi. 15Ikakhala kwa ndande ya chakudya m'bale wako wadandaula, siwendancho pakati pa chikonano. Usadamuwananga kwa chakudya chako munthu uyo ka ndande yake Kristo madafa.16Chimwecho msadalamula vichito vanu vabwino sividachiticha wanthu kwaesela. 17Pakuti ufumu wa Mulungu osati kwa ndanda ya chakudya ndi kumwa, nampho kwa ndande ya haki, mtendele, ndi chisangalalo pakati pa Mzimu Oyela.18Pakuti iye wamtumikila Kristo kwa mtundu uu wavomeleka kwa Mulungu ni wavomeleka kwa wanthu. 19Kwa chimwecho basi, tichate vinthu va mtendele ndi vinthu ivo vimjenga munthu mwina.20Usadawananga nchito ya Mulungu kwa ndande ya vakudya. Vinthu vonche kwa chazene ni vabwino nampho ni kuipa kwa munthu yujha wakudya ndi kuchiticha iye kujikuwala. 21Ni bwino kusiya kudya nyama, kapena kumwa divai, kapena chalichonche icho chimenecho m'bale wako wadandaulichidwa.22Ichi chikhulupi icho ulinacho, chiike pakati pako wamwene ndi Mulungu. Wapachidwa mwawi yujha siwajhilamula mwene pakati pa chijha wachivomela. 23Uyowali ndi mantha walamulidwa ikakhala wakudya, kwa ndande siichokela ndi mtendele. Ndi chalichonche ichosichichokela ndi chikhulupi cha machimo.

Chapter 15

1Chipano ife tili ndi mphavu ifunika kuutenga udhaifu waanyiyao adhaifu ndi sifuni kujikwadilicha tawefe. 2Kila mmoji watu wamkwadiliche jirani wake kwani ndi chinthu chabwino, lengo la kumuyaluza.3Kwani ata Kristo siwadajidiliche mwene. Badala yake idali ngati umo idalembedwa, matukwano yawaja adakutukwana yanipeza ine. 4Kwa chalichonje chidachogolela kulembedwa chidalembedwa katielekeza, kwakusudi kuti kupitila uvumilivu di kupitila kutilidwa mtima ndi malembo tidakala ndi ujasili.5Chipano Mulungu wa uvumilivu ndi wakutila mtima akupacheni kukala ndi nia sawa kwa kila mmoji kulingana ndi Yesu Kristo. 6Wakoze kuchita chimwecho kwa nia imoji tikoze kumtukuza kwa mkamwa mmoji Mulungu ndi Ambuye wa bwana watu Yesu Kristo. 7Kwachimwecho mlandileni kila moji, ngati muja Kristo wadakulandilani, kwa chimwemwe cha Mulungu.8Ngati nikamba Kristowadachitidwa mtumiki w tohara kwa niaba ya uzane wa Mulungu. Wdachita chimwecho ili kuti wakoze kusibitisha ahadi zidachochedwa kwa mababa. 9Ndi kwa majiko kumtukuza Mulungu kwa chisangalalo chake, ngati umo yalembedwa, "kwachimwecho sinichoche si sifa kwako pakati pa jiko ndikuimba sifa katika jina lako."10Kuna ikamba, sangalalani, anyaimwe ajiko pamoji ndi wantu wake. 11Tena "mtukuzeni Ambuye, anyaimwe wantu wa jiko lonche, sia wantu ajiko lonche amtukuze iyo."12Tena Isaya wakamba, "sikukale ndi shina la Yese ndi mmoji siwainuke kutawa pakati pa mataifa. Siakale ndi matumaini katika iye"13Chipano Mulungu watumaini akondweche ndi chisangalalo yonche ndi amani kwa kuamini, ili kuti mukoze kuchita katika imani kwa mphavu ya Roho Mtakatifu.14Ine namwene nane nashawishidwa namwe abale wanga nikushawishini kuti, namwe mkoza kuhimizana kila mmoji ndi mnjake.15Nampho nilemba kwa ujasili zaidi kwanu pamwamba pa vichito fulani ili kwakumbuchancho chifuko cha kipawa icho napachidwa ndi Mulungu. 16Chipawa ichi chidal kuti nikoze kukala mtumii wa Yesu Kristo wadatumidwa kwa jiko, kujichocha ngati kuhani wa injii ya Mlungu, nikadakoza kuchita chimwecho ili kujichocha kwanga kwa jiko kukale kwavomelezedwa; kwabagulidwa ndi Mulugu kwanjila ya Roho Mtakatifu.17Kwachimwecho chisangalalo changa chilipo katika Kristo Yesu ndi katika chinthu cha Mulungu. 18Ngati sindikoza kusubutu kukamba lalilonche ingakalr kuti Kristo wakwaniza kupitila kwanga utii wajiko ivi vintu vakamilika kwa mau ndi chinthu. 19Kwa mphavu za ishara ndi maajabu ndi kwamphavu za Roho Mtakatifu jiko chikala kuti kuchoka Kuyerusalemu ndi kuzungulia kwa kuali ngati iliko ndioza kuitenga kubwalokwa ukamilifu injili ya Kristo.20Kwa njia ino, chifuko changa idakakala kutangaza injili, nampho pamal Kristo wajiwika kwa jina ili kuti sinikoza kumanga pamwamba pamsingi wa munthu mwina. 21Ngati umoidalembewa, ambao kwa iye walibe nkhani zake wdaja siwaone, ndi waja ambao siwadavele siwaiwe.22Kwachimwecho nidali nachekelezedwa nyengo yambili kuja kwanu. 23Nampho chipano, nilibevecho pamalo paliponche katika maiko ndi nidali ndidakumbila kwa vyaka vambili kuja kwanu.24Kwachimwecho nyengo zonche nikapita pania, nikulupalila kuwaona ndi kapita ndiukoza kupelekedwa njila yanga ndi anyaimwe, pambuyo pakukala ndi chisangalalo ushirika ndi anyaimwe kwa muda.. 25Nampho chipano ndipita Kuyerusalemu kwahudumia waumini.26Chifuko idawakwadilicha wantu wa Makedonia ndi wadakusanya changizo maalumu osauka pakati pa waumini. 27Nde umo idali ka upendo wao. Ndi hakika, ali ndi deni wao, maana ikakala mataifa ashiriki katika vinthu vao va kiroho, adaidwa ndi nao kwahudumia katika mahitaji ya vinthu.28Kwachimwecho, ntawi nakwaniza ichi ndikukala ndi kukwaniza wa tunda ili kwao, ine sinipite mnjila palimoji namwe kumeneko Kuhispania. 29Ndijiwa kuti ntawi nikaja kwanu, sinije kupitila akamitali ka ba baraka za Kristo.30Chipano kumtondo naabale kwa Ambuye watu Yesu Kristo, ndi kwa chikondi cha Roho, kuti mkusanyike pamoji nane kupitila mapemphelo yanu kwa Mulungu ndi kwachifuko changa. 31Pemphani kuti nikoze kulamichidwa kuchoka kwa waumini. 32Pemphani kuti nikoza kuja kwanu kwa chiangalalo kupitila mapenzi ya Mulungu ndi kuti ndikoza kukala pamoji namwe, kupeza kupumulila.33Ndi Mulungu wa amani wakale pamoji namwe mwaonche. Amina.

Chapter 16

1Naleka wanu Fibi mlongo watu, iye wali mtumiki wa kanisa ilo lili Kenkrea. 2Kuti mkoza kumlandila kuchokana ni Mpululusi itani chimwechi katika mutu wa ntengo wa okulupalila, ni muime pamoji ni iye kwa lalilonche ilo siwakale ni kulifuna kwa ilo. Chifukwa iye mwene wakata otumia wa Ambili, ni kwa ajili ya ine namwene.3Mlonjeleni Priska ni Akila, achita nchito pamoji ndi ine katika Mpulumusi. 4Kuti kwa umoyo wanga adayoika poipa umoyo wao achinawene. Nichocha mayamiko kwa anyiiwo ndi osati inepe, bali ni makanisa yonche ya jiko. 5Lilonjele kanisa ilo lili kukomo lao. Mlonjele Epanieto okondedwa wanga, uyo wali obadwa oyambila wa Mpulumusi katika Asia.6Mlonjele Mariamu uyo wachita nchito kokazana chifuko chanu. 7Mlonjele Androniko ni Yunia, apafupi wanga ni omangidwa pamoji ni ine. Ni amate pamoji ni opusila, pamoji ni anyiyao adachogolela kumjiwa Mpulumusi kumbuyo kwanga. 8Msalimie Ampliato , okondedwa wanga katika Ambuye.9Msalimie Urbano, ochita nchito pamoji ni ine katika Mpulumusi, ni Stakisi okondedwa wanga. 10Mlonjele Apele, uyo wavomeleka katika Mpulumusi. Mwalonjele onche anyiyao ali katika nyumba ya Aristobulo. 11Mlonjele Herodioni bwenji langa. Nilonjelele onche ali katika nymba ya Narkiso, anyiyao ali katika Ambuye.12Mlonjle Trifaina ni Trifona, achita nchito kojituma katika Ambuye. Mlonjele Persisi okondedwa uyo uyo wachita nchito yaikulu kwa Ambuye. 13Mlonjele Rufo, wasankhidwa katika Ambuye ni mame wake ni anga. 14Mlonjele Asinkto, Flegon, Herme, Patroba, Herma na achabale onche ali pamoji ni anyiio.15Mlonjele Filologo ni Yulia, Nerea ni Mlongo wake ni Olimpa ni okulupalila onche ali pamoji ni anyiio. 16Nilonjeleleni kila mmoji kwa busu loyela. Makanisa yonche katika Mpulumusi yakulonjelani.17Chapano nikupemphani, achabale kuganizila juu ya anyiyao achila mkanganyo ni kukinga. Apita kumbuyo ni mayaluzo ambayo yayojiyaluza ng'anamukani mchoke kwao. 18Chifuko wanthu ngati anyiyawa samtumikila Mpulumusi Ambuye, bali mimba zao achinawene kwa mau yao yolainika ni kukuelekela kwa unami anyenga mitima ya nyiyao sadalakwe.19Kwa chifani cha ulemu wanu mwamfikila kila mmoji. Kwa icho, nisekelela juu yanu, nampho nikufunani anyiimwe mkale ni njel katika maisha ya ubwino, ni simdakala ni kulakwa pakati pa voipa. 20Mlungu wa mtendele siwachedwa kumpweteka oipa.21Timotheo, ochita nchito pamoji ni ine, wakulonjelani, ni Lukio, Yasoni ni Sospeter, achabwenji wanga. 22Ine, Tertio, nalemba mau ili, nikulonjelani katika jina la Ambuye.23Gayo uyo wanipenyelela n kwa kanisa lonche likulonjelani. Erasto, openyelela vyuma va muji, wakulonjelani, pamoji ni Kwarto mbale watu. 24(Mwawi wa Ambuye Mpulumusi ukale namwe mwaonche. Amina.")25Chapano kwa iye wali mphavu kuchika muime kuchokana ni mau ni mayaluzo ya Mpulumusi kuchokna ni malangizidwe ya chobisika chabisika kwa nyengo yaitali. 26Nampho saino yatovunukulidwa ni kuita kujiwikana ni malembo yaganizilidwa kulingana ni lamulo la Mulungu wa Muyaya, kwa ulemu wa chikulupi mkati mwa maiko yonche?27Kwa Mulungu yoka wali njelu, kupitila Mpulumusi, kukale ni ufulu nthawi yonche. Amina.

1 Corinthians

Chapter 1

1Paulo, uyowatanidwa ndi Kristo Yesu mtumiki kwa chikondi cha Mulungu, ndi Soathene m'bale wantu. 2Kwa kanisa la Mulungu ilo lili ku Korintho, kwa anyiwaja anyiyawo aikidwa wakfu mkati mwa Yesu Kristom anyiyawa atanidwa kunkala wantu oyela. Talembela ncho anyiwaja onche alitana jina la Ambuye wanthu Yesu Kristo pakati pa pamalo panche, Ambuye wao ndi wantu. 3Neema nmdi nchisangalalo chikale kwanu kuchoka kwa Mulungu tate wantu ndi Ambuye wantu Yesu Kristo.4Siku zonche ndi muyamikila Mulungu wanga ndande yanu, ndande ya neema ya Mulungu ambayo Kristo Yesu wakuninkani. 5Wakuchitani mkale opata pakati pa kila njila pakati pa kamba ndi pamaji ndi njelu zonche. 6Wachita opata, ngati oshuudia kuhusu Kristo kuti wasibitishida kuti kuti uzene mkati mwatu.7Chipano simchepekelo dwa vichito vya mizimu, ngati umo mulindi hamu yakundilndilila kumasulidwa kwa Ambuye wantu a Yesu Kristo. 8Siwakwamulileninchoni anyiimwe hadi pontela, ili simdandaumilidwa siku ya Ambuye wantu a Yesu Kristo. 9Mulungu ndi wauzene ambaye wadakutanani anyiimwe pakati pogwilizana ni mwana wake, Yesu Kristo ambaye wantu.10Chipano ndikupembani achikaka ndidada zanga, kupitila jina la Ambuye watu a Yesu Kristo, kuti wonche muomele, ndi kuti kusidakala ndi magulumagulu mkati mwanu. Ndikupembeni kuti mgwilizanepamoji ndi ganizo limoji ndi kupitila mpango mmoji. 11Kwani wantu wanyumba ya Kloe anifotokozolela kuti kuti magulumagulu mkati mwanu.12Ndili ndi maana ii; kilammoji wanu wakamba, "ine Paulo, "au" ine ndi wa Kefa "au" ine ndi wa Kristo." 13Bwa! Kristo wagawidwa? Bwa! Paulo wawambidwa kwa chifukwa chanu? Bwa! Mdabatizidwa kwa jina la Paulo?14Mdimyamikila Mulungu kuti sindida mbatize waliyonche, ingakale Krispo ndi Gayo. 15Ii idalikuti palibe waliyonche wadakakamba mdabatizidwa kwa jina langa. 16(Nampho n ndidabatiza anyumba ya Stephania. Zaidi ya pamenepo, sindijiwa ngati ndidabatiza munthu mwinancho waliyonche).17Pakuti, Kristo siwadanitume kubatiza ila kukambilila mau la Mulungu. Siwadanitume kukambila kwa mau ya chilungama ya binadamu, ili kuti mphavu ya mtanda wa Kristo usidachochedwa.18Pakuti ujumbe wa mtanda ndi upuuzi kwa anyiwaja akufa. Nampho kwa anyiwaja ambao Mulungu walamicha, ndi mphavu ya Mulungu. 19Pakuti zalembedwa, "sindiwananga chilungamo cha anyiwaja wene chilungamo. Sindiwanange kujiwa kwa wene njivu."20Wali kuti munthu mwene chilungamo? Wali kuti munthu mwene njeru? Wali kuti akamba ko shawishi kwa pajiko pano? Bwa Mulunu siwaigeuze hekima za jiko ili kukala ujinga? 21Tangu jiko lakala mkati mwa hekima yake siida mjiwe Mulungu, idamkondwecha Mulungu pakati pa ujinga wao wa kukambilila ili kulamicha anyiwaja akulupalila.22Kwa Wayahudi afunchi la chifanizi cha vadabwi cha ndi kwa Wayunani afunafuna hekima. 23Nampho tukambilila Kristo wadwabidwa, wali chikwazo kwa Wayahudi ndi ujinga kwa Wayunani.24Nampho kwa anyiwaja atanidwa ndi Mulungu, Wayahudi ndi Wayunani, tumkambilila Kristo ngati mphavu ndi hekima ya Mulungu. 25Pakati ujinga wa Mulungu uli ndi hekima kuliko ya wanadamu, ndi uzaifuwa Mlungu uli ndi mphavu zaidi ya wanadamu.26Penya kutanika kwa Mulungu pa mwamba panu, kaka ndi dada zanga, osati ambili wanu mdai ndi hekima mkati mwa vichito va wanadamu. Osati ambili wanu adali ndi mphavu. Osati ambili wanu mdabadwa mkati mwa ufulu. 27Nampho Mulungu wadasankhula vinthu vijinga vya pajiko ili kuviwewelecha va hekima. Mulungu wadasankhula icho chi zaifu pakati pa jiko kuchiwewelecha cha mphavu.28Mulungu wadasankhula chija chilindi hali ya panchi ndi chiwewelengedwa pajiko. Wasankhula ata vinthu ivo sividawelengedwe kuti ndi vintu, kwa kuvichita osati vinthu vili ndi mtengo. 29Wadachita mchimwecho ile wasadakalapo waliyonche wali ndi ndande ya kuokoledwa.30Ndande ya chija Mulungu ichowachita, chipano muli mkati mwa Kristo Yesu, ambayo wachitika hekima ndande yanthu kuchoka kwa Mulungu wadalimalinga yatu ubwino ndi kulamicha. 31Ngati matokeo, ngati mau umalikambila, "uyo wajisu, wajisifu mkati mwa Ambuye."

Chapter 2

1Yapo ndidafika kwanu akuuwanga ndi alongo wanga sindidaje ndi mau yosongozela ndi ya ubwino ngati umo ndidalalikila uzene uwo udabisika pakati pa Mulungu. 2Sindafune kujiwa chilichonche yapo ndidali mkati mwanu ikapanda Yesu Kristu ndi iye wadawambidwa.3Ndidali ndi anyaimwe pa kudwala, ndi mkati mwa Martha ndi pakutetemela kupunda. 4Utenga wanga ndi kulalikila kwanga siku dali mkati mwosongozela ndi ulemu, pambuyo pake idal kujiwicha mzimu ndi mphamvu. 5Kuti kulupi lanu lisakala mkati mwa ulemu wa wanthu, ikapanda ndi mkati mwa mphamvu ya Mlungu.6Nyengo ino tikamba ulemu mkati mwa wanthu wa akuluakulu, nampho osati ulmu wa jhiko lino kapena olamula nyengo ino. Anyiyao apita. 7Pambuyo pake tikamba ulemu wa Mlungu mkati mwa uzene osabisike, ulemu udabisika iyo Mulungu wadasankha pambuyo pa ulembelelo wathu.8Palibe olamula waliyonche nyengo ino uyo wamajiwa ulemu uwu, nyengo zijha ngati amakajhiwa sadaka azunja Ambuye aulemelelo. 9Ngati umo yalembedwela, vinthu ivo diso silida penye palije kuthu ilo lidavela maganizo siyadaganize, vinthu ivo Mulungu wadavipanga kwa anyiyao amamkonda iye.10Ivinde vinthu Mulungu wadatambasula kwathu kupitila mzimu, pakuti mzimu uona kila chinthu, ingakale vinthu va mkati mwa Mulungu. 11Ndande yani wajhiwa maganizo ya munthu. Ikapanda mzimu mu mtima mwake? Kwaicho palijhe uyo wajhiwa nkhani za Mulungu. Ikapanda mzimu wa Mulungu.12Nampho sitidalandile mzimu wa jhiko, nampho mzimu uo wachokela kwa Mulungu kuti tikozen kujhiwa kwa ufuru nkhani tapachidwa ndi Mulungu. 13Tikamba nkhani izi kwa mau yayon ya ulemu wa munthu siyakhoza kuyaluza. Nampho mzimu utiyaluza, mzimu udatambasula mau ya mzimu kwa ulemu wa mzimu.14Munthu osati wa Mzimu siwalandila nkhani za mzimu wa Mulungu. Pakuti yameneyo ndi uchitekwa wake, siwakoza kujhiwa ndande yajhikana kimzimu. 15Iye wa mzimuwalamula nkhani zonche. Nampho walamulidwa ndi wina. 16"Yani wakhoza kujhiwa maganizo ya ambuye yayowakhoza kuyaluza iye?" Nampho tile ndi maganizo ya Kristu.

Chapter 3

1Ndi ine, kaka ndi dada zangu, sinidakambe ngati anyiimwe wandu kimzimu, nambo ngati wandu kitupi ngati wana wangono pakati pa Kristo. 2Ndikaku mwechani likama ndi opande nyama, pakuti simudali tayali kwakuja nyama ndi mbaka chapano si muli tayali.3Pakuti anyiimwe mukali kitupi pakati njaje ndi kujiona yaonekana pakati panu, bwa, simulama kulingana nditupi ndi bwa, simuenda nati umoifunikilana mundu? 4Pakuti mmoji wakamba, "nimchata Paulo" ndimwina kukamba, "mchata Apolo," najichita ngati wandu? 5Paulo ndi yani? Ndi Paulondiyani? Otumidwa ayuja muda mkulupilila, pakila chindu icho Ambuye adamnikha njito.6Ine nidavyala, Apolo wadatila maji nambo Mulungu wadayakulicha. 7Pa icho, palibe uyo wadavyala wala kutila maji walibe chilichonje nambo Mulungu wakulicha.8Chopano uyo wavyala ndi watila maji onje sawa, ndi kila mmoji si walendile zawadi yake kulingana ndi njito yake. 9Pakuti ife ndi ogwila njito ya Mulungu anyiimwe ni bustani ya Mulungu munda wa Mulungu.10Kuchokana ndi nema ya Mulungu ni daningidwa ngati omanga pamwamba pake. 11Pakuti palibe mwina wakoza kumanga msingi wina poposa uwo wamanga uwo uli Yesu Kristo.12Chopano ngati mmoji wanu wamanga pamwamba pake ka dhahabu kulama naye yadhamani, mitengo maufu, pena machamba. 13Jito yake simasulidwe pamwamga wausana siukambilie. Pakuti siukambilile ndi moto siuye se ubwino wanjito wakila mmoji icho wachita.14Ngati chilichonche mundu wadamanga sichi kale. Iye siwalandile mboto. 15Nambo ngati jito ya mundu ika pyelela kwa moto, siwapate asara. Nambo iye mwene siwaokoledwe ngati vija kupukwa pamoto.16Siujiwa kuti anyiimwe nyumba ya Mlungu ndi kuti Roho ya Mulunu ikala mkati mwanu? 17Ngati mundu siwaliwanange nyumba ya Mulungu siwamuwanange mundu yuja. Pakuti nyumba ya Mulungu ndi yoelesedwa, ndi anyiimwe namwe.20Mundu wasadanyi nyenga mwene, ngati walienje pakati panu wakhaniza wali ndi ulemu pandawi ino, wakale ngati "chilekwa" nde siwakale ndi ulemu. 19Pakuti ulemu wa jiko lino ndi ujinga pakati pa Mulungu, pakuti yalembedwa, "lakodwecha ali ndi ulemu pachila zao." 18Ndiposo "ambuye ajia makhanizo yao ya ali ndi ulemu ndi mtila."21Chocho mundu wadamkulupilili mundu pakuti vindu vonji ndi vanu. 22Ngati ndi Paulo, kapena Apolo, kapena Kefa, kapena dunia, kapena maisha, kapena nyifa, kapena vindu vilip, kapena ivo sivikalepo. Voje ndi vanu, 23namwe ndi a Kristo ndi Kristo ndi wa Mulungu.

Chapter 4

1Chimwechi ndimo muntu ifunika watiwelenge ife ngati ngati ogwila nchito a Kristo ndi ndiofaniza kusunga siri za uzene za Mulungu. 2Pakati paili, chifuniko pakusunga siri za Mulungu ndikuti osunga wa kale okurupalika.3Nampo pakati paine ni chintu cha ching'ono kupuda kuti ndi lamulidwa pamoji ndi anyiimwe kapena kulamulidwa kwa chimuntu pakuti sindijilamula namwene. 4Sindi lamula namwene, iyi ilijemate kuti ine ndili wa mate, ndimulungu walamula.5Kwa mwemo msada kamba lamulo pamwamba pa chilichonche pambuyo pakubwela kwa Mulungu siwajenalo poyela nkani zajibisa, kumdima ndi kuvunukua chifumo cha mitima. Nde pamene waliyenche siwalandile utemeleli wake kuchokela kwa Mulungu.6Chapano anyamate ndi anauwaliwanga ine namwene wake ndi Apolo nndaitumikila mteteuu chifuko chano dale kuti mujiyaluza mate ya makambidwe, "usadapita kupunda kwa mmene yalembedwela." Ii ni kuti palije mmoji wanu wo sichita pamwamba pawina. 7Mate yani wapenya ngati sindim pakati panu ndimwena? Chiyani chimene ulije siuda chilandile chabe? Ngati watolandila chabe chifuko chiyani mjichita ngati simdachite chimwecho?8Chazene mlinavo voncheivo mmavifuna! Chazene mwato kuwina! Mwayamba kulanile lila ndi kuti muli ndi vinthu kupunda ife! Zene ndikufuni kulamulila pamoji nano. 9Kwaicho ndiganiza Mulungu watiika ife utumidwa wake ngati kutilangiza wotela pakati panzele okalila limoji ndi ngati wntu alamulidwa kupedwa. Takala ngati hikondwelelo kwajiko, pa angelo ndi kwa wantu.10Ife palibe maganizo yabwino pakati pa Kristo nampo anyiimwe muli ndi ulemu pakati pa Kristo, tulibe mtendele nampo anyiimwe muli ni mphavu mlemekezedwa, nampho ife sipepulidwa. 11Ata ntawi ino tili ndi njala ndi hiyo tiaje nchalu tabulidwa ndi sonjincho tiliche malo yokala.12Tichita nchito ka mtima ndi manjan yatu ta achinawene yapo ti siyakulemekezedwa tipeleka mwawi, yapo tipeza mavuto tivumiwa. 13Yapolitukanidwa tibwezela kwa mtima ochika tili, ndi tikali tiwelengedwa nngati kuti kukanidwa ndi jiko ndi zinyalala kwa vichito vonche.14Sindilemba nkani izi kukuchitani chipongwe anyiimwe nampo kukabwelani anyiimwe ngati wana wanga ndi kukondani. 15Atangati muli ndi akulangyaluzani makumi yambili pakati pa Kristo mulije achaatate ambili. Chifuko ndili tata wano kupitila Kristo kupitila mau la Mulungu. 16Mmwemo ndi kupemphani muni lanje ine.17Mmwemo nde mateyake ndida mtumza kwanu Timotheo okondedwa wanga ndi mwana ukurupalika pakati pa Mulungu siwakukumbuchani njila zanga pakati pa Kristo ngati mmene ndi mayaluzila pamalo paliponche ndi nnyumba ya Mulungu iliyonche. 18Chapano ochepa pakati pano ajiika pamwamba achita ngati sindibwelancho kwa nyaimwe.19Nampo sindilobwelancho kwanu posachedwapa, ngati Mulungu siwalonde pamenepo sindije osati kwa mau yao tu achawene ajikweza nampo sindizione pavu zao. 20Pakuti ufuru wa Mulungu siukala pakatikati pamau ikapanda pakati pa mpavu. 21Mifuna chiyani? Ndije kwanu ndi chiboko kapenna kwa chikondi ndi pakati pamtima wa chika?

Chapter 5

1Tavela nkani kuti kuli chigololo mmoji wa anyiimwe, ntundu wa chigololo ivho palijenepo ata pakatikati pa wandhu ajhiko. Tili ndi nkhani kuti mmojhi wa anyiimwe wagona ndi mkazi wa atate wake. 2Namwe lewajhikweza! Pamalo pa kudandaula? Yujha wadachita chimwecho waifunika kuchochedwa mwa anyiimwe.3Ingakale sinili pamojhi namwe chitupi nampho nili namwe chizimu, nato mlamula iye wachita ivi, ngati nidalipo. 4Yapomsoganika pamojhi pa jhina la Ambuye watu Yesu ndi Mzimu wanga uli pambajhe ngati kwa mphavu za AMbuye watu Yesu, nato mlamula mundhu mmeneyo. 5Nato mpacha mundhu mmeneyo kwa satana kuti tupi lake liwanangidwe kuti mzimu wake ukoze kupulumuchidwa pa siku ya Ambuye.6Majivuno yanu osati chindhu cha bwino. Simujiwa kuchuchuluka pang'ono kuwananga yaniphumbu? 7Jichukeni anyiimwe mwachinawene kuchuchuluka kwa kale kuti mukale donge la chipano, kuti mkale mkate uwo siudachuchulidwe. Pakuti Kristo mwana wa Mbelele watu wa Pasaka watachinjidwa. 8Kwa icho tiikondwele karamu osati kwa kuchuchulika kwa kale, kuchuchuluka ya ukalo oyipa ndi voipicha pamalo pake tikondwele ndi mkate uwo siudatilidwe kuchachulidwa kw kujichicha ndi zene.9Nidalemba pa kalata yanga kuti msadachatana ndi achiwelewele. 10Ndilibe mate achiwelewele ajhiko lino, kapena ndi anyiyawo okumbila kapena olanda kapenaolambila vosepa kwa kukala papatali nawo, basi idakafunika mchoke pajhiko.11Nampho chipano nikulembelani msadajisingizana ndi waliyencheoyo watanidwa mkulu wanga kapena mlongo wanga pa Kristo. Nampho walama pa chiwelewele kapena mmeneyo okumbila kapena olandalanda, au olambila vosepa kapena otukwana kapena wamowa! Kapenapo msadwa naye mundhu wa mtundu umeneo. 12Kwa icho sindiwandikile bwenji kuwalamule anyiawo alikubalo kwa kanisa? Pambuyo pake, anyiimwe simdalamule ali mkati mwa kanisa? 13Nampho Mulungu walamula alikubwalo, "mchocheni mundhu oyipa mmojhi mwa anyiimwe."

Chapter 6

1Mmoji wanu yapowakala ndi vuto ndi mnjake, waijesa kupita kukoti la opande malinga osati ngati pachogolo pa okulupilila 2Semjiwa okulupilila sange jiko la panchi? Ni ngati simlilange jiko la panchi, simkoza kulamula vinthu vopande mate? 3Simjiwa kuti sitialange angelo? Kwa mtundu wanji tikoza kulamula vintu va umoyo uu.4Ngati tikoza kulanga vinthu va moyo uu, ndande chiyani muyesa kupeleka mlandu pachogolo pa yao saima mkanisa? 5Nikamba ivi kwa nchoni yanu. Palije wali ndi njelu pakati panu uyo wakwana kuika vinthu bwino pakati pa m'bale ndi m'bale. 6Nampho ngati umo ili chipano, okulupilila mmoji wapita kukoti chifukwa cha okulupilila mwina, ndi mlandu kuiika pachogolo pa olamu kukoti osakulupilila.7Uzene ndi kuti pali kuchepekela kwanu, kuti muimbilana mlandu mwachinawene, mate simbasa kudyeleledwa? Si mbasa kulandidwa chuma chanu? 8Nampho anyiimwe nde mdyelela ndi kulanda chuma mwachilila mbaka achiabale wanu.9Bwa simjiwa kuti wanthu oipa saasilidwa ufumu wa Mulungu msajinyenga, mahule saasilidwa udfumu wa Mulungu ingakale olambila chosepa, achigololo, kenaka ogonana achimu na ndithu. 10Ankhungu, okumbila olonjela, otukwana ndi olanda wanthu kwa mphavu. 11Akumoji mdali chimwechi, nampho mdaelechedwa, nampho mdawelengedwa malinga pa jina la Ambuye Yesu Kristo ndi mwa mzimu waMulungu watu.12Vinthu vonche ni voenela kwanga nampho asati vonche va mate, vinthu vonche ni voenela kwanga, nampho ine sinikala panchi pa chinthu chilichonche. 13Vakudya ndi kwa mimba ndi mimba kwa vakudya nampho Mulungu siwavichoche vonche viwili, mimba ndi vakudya, nampho tupi osati kwa chigololo nampho kwa Ambuye, ni Ambuye kwa tupi14Ndi Mulungu wadakahyucha Ambuye satihyushencho ife pa mphvu zake. 15Bwa simjiwa matupi yanu ndi viwalo va Kristo, ntenge viwalo va Kristo ndi kuvichita viwalo va hule? Iyai.16Simjiwa uyo walunjidwa ndi hule walitupi limoji ndi uleyo? Ngati umo yakambila malembo, "awili saakale tupi limoji." 17Nampho uyo wachinjana ndi Ambuye wakala mzimu umoji ndi iye.18Chitaweni chigololo chimo lililonche wachita munthu wachita kubwalo kwa tupi lake nampho uyo wachita chigololo eachita mkati mwa tupi lake mwene.19Simjiwa kuti matupi yanu ni kanisa la mzimu oyera, wakala mkati mwanu, yuja mdapachidwa kuchoka kwa Mulungu ? Simjiwa kuti osati mwachinawene? 20Kuti mdagulidwa kwa ntengo. Kwaicho mkuzikeni Mulungu kwa matupi yanu.

Chapter 7

1Kukhuza nkhani iyomdanilembela: kulinyenga iyo iliyobwino wammuna wasidaghona ndi mkazake. 2Nampho kwa ndande ya maeso yambili ya chitole kila wammuna wakhale ndi mkazake, ndi wamkazi wakhale ndi mmunake.3Wammuna wafunika kumpacha wamkazi haki yake ya ukwati, ndi richimwecho, wamkazi naye kwa mmunake. 4Opande wamkazi wal ndi malamulo pakati pa thupi lake, ndi wammuna. Ndi nchimwecho wammuna naye walibe malamulo pakati pa thupi lake, nampho wamkazi walinayo.5Msidamanana yapomghona pamojhi, ikakala mwavomelezana kwa nyengo iyoifunika, chitani nchimwecho kupta nyengo ya mapemphelo. Pothela mukhoza kubwelelanancho pamojhi, kuti satana siwadaajha kukuyeselani kwa kiasi. 6Nampho nikamba nkhani izi kwa kufuna kwanga ndi opande ngati lamulo. 7Nikhumbila kila mmoji wadakakhala ngati ine umonili. Nampho kila mmojhi wali ndi mphoto yake kuchoka kwa nMulungu. Uyu wali ndi mphoto nndi yujha wali ndi mphoto nimeneyo.8Kwa osakwatiwe ndi ofedwa ndi achamunao nikamba kuti, ni bwino kwaanyaio ngati akakhala bila kukwatiwa, ngati umonili ine. 9Nampho ngati sakhoza kujhichekeleza. Afunika kukwatiwa. Pakuti mbasa kwao kukwatiwa kuliko kukhala ndi khumbilo.10Chapano kwa anyiyao akwatiwa napacha thauko, opand ine nampho ni Ambuye. "Wamkazi wasi danasiana ndi mmunake." 11Nampho ngati wakajhipatula kuchoka kwa mmunake, wakhale chimwecho bila kukwatiwa au mwina wake wavane ndi mmunake. Ndi, "wammuna wasidampacha kalata mkazake."12Nampho kwa anyiyao akhala, ni kama-ine, opande Ambuye kuti ngati m'bale waliyonche wali ndi wamkazi osavomele ndi kuvomela kukhala naye, wasidamsia. 13Kama mwanamke ana mme asiyeamini, na kama anaridhika kuishi naye, asimwache. 14Kwa wammuna uyosiwavomela wachukidwa kwa ndande ya mmunake uyowavomela. Valivonche wana wanu adakakhala osati bwino. Nampho kwa chazene achukidwa15Nampho mnjako uyo siwavomela wakachoka wachoke. Kwa mate imeneyo, kaka kapena dada siwamangidwa kwa vilanga vao. Mulungu watitana ilame kwa mtendele. 16Ujiwa bwanji ngati wamkazi, kuti siwamlamiche mmunake? Kapena ujhiwa bwanji ngati wammuna kuti siwalamiche mkazake.17Kila mmojhipe walame ngati Ambuye umoadakugawilani, kila mmojhi ngati Mulungu umowadaatanila anyaio. Uku ni kuchogoza kwanga kwa makanisa yonche. 18Walipo uyowadaumbalidwa uyo wadatanidwa kuvomela? Siwadaesa kuchocha chidindo cha umbalo lake. Walipo waliyonche uyowadatanidwa pakati pa mtendele siwadaumbalidwe? Siafuka waumbalidwe. 19Kwa ili kuti waumbalidwa kapena siwadaumbalide popande mavuto. Icho chili ndi mavuto ni kuvomela malamulo ya Mulungu.20Kila mmojhi wakhale pakati pa kutanidwa umo wadali yapowadatanidwa ndi Mulungu kuvomela. 21Udali kapolo nyengu Mulungu yapo wadakutana? Usaganiza kukhuza limenelo. Nampho ngati ukhoza kukhala huru chita n'chimwecho. 22Kwa mmojhi uyowadatanidwa ndi Ambuye ngati kapolo ni munthu huru pakati pa Ambuye. Ngati mujha, mmojhi wali huru yapo wadatanidwa kuvomela ni kapolo wa Kristo. 23Mwathogulidwa kwa mtengo, chimwecho msadahala akapolo wa binadamu. 24Anyakaka ndi anyadada wanga, pakati pa kulama kwalikonche kila mmojhi wathu yapotidatanidwa kuvomela, tikhale ngati chimwechijha.25Chipano, anyiwajha onche yaosiadakwate, nilibe lamulo kuchoka kwa Ambuye. Nampho nikupachani maganizo yanga ngati umonili. Kwa lisungu la Ambuye ilolivomeleka. 26Kwa chimwecho, niganiza chimwecho kwa chifuko cha kujchauchika, ni bwino wamuna wakhale ngati umo wali.27Wamangidwa kwa wamkazi kwa chilanga cha ukwati? Usidfuna lisungu kuchoa kwa limenelo uli ndilisungu kuchoka kwa wamkazi kapena siudakwatiwe? Usadafunafuna wamkazi. 28Nampho ngati ukakwata, siudachite machimo, ndi ngati wamkazi siwadakwatiwe wakakwatiwa, siwadachite machimo. Akali wajha akatana kupata kuchauchika kwa mtundu ndi mtundu ndi ine nifuna nikupembenuzeni yameneyo.29Nampho niamba chimwechi, anyakaka ndi anyadada wanga, nyengu ni yaifupi, kuyambla saino ndi kuendekela, anyiwajha ali ndi wachikazi ajhilama ngati alibe. 30Onche ali ndi lisungu ajhichite ngati adali opade lisungu, ndi onche yaoasangalala, ngati adali osasangalala, ndi onche agula chinthu chalichonche ngati chalichonche. 31Ndi onche yao aendela ndi za jhiko akhale ngati saendela nalo. Pakuti mithethe ya jhiko ifikila pothela pake.32Nifuna mukhale huru kwa kuchauchika konche. Wammuna uyo siwadakwate wajikhuzicha ndi vinthu ivovimkhuza Ambuye mtundu wa kumkwadilicha iye. 33Nampho wammuna uyowakwata wajhikuzicha ndi nkhani za jhiko, mtundu wa kumkwadilicha mkazake, 34wagawikana. Wamkazi uyosiwadakwatiwe kapena bikila wajhikuzicha ndi vinthu kukhuza Ambuye mtundu wa kujhigawa pakati pakati pa tuphi ndi pakati p mzimu. Nampho wamkazi uyowakwati wa wajhikuzicha ndi vinthu va jhiko, mtundu kumkwadilicha mmunake.35Nikamba chimwechi kwa pindu mmwachinawene, ndi siniika msampha kwanu. Nikamba chimwechi kwa ndande ni haki, kuti mukhoza kukhala wakfu kwa Ambuye popande chijhinchi chalichonche.36Nampho ngati munthu waganiza siwakhoza kumchitila kwa ulemu mwali wke, kwa ndande ya kuganiza kwake kuli ndi mphavu kupunda, siyawakwatane nae ngati umowakondela, opande machimo. 37Nampho ngati wachita malamulo kusiyakutwta, ndi kulibe ndande ya thauko, ndi ngati wakhoza kuilamula hamu yake, siwachite bwino ngati siwamkwata. 38Chimwecho uyowamkwata mwali wa chita bwino, ndi wliyonche uyowasankhula kusiya kukwata siwachite bwino kupunda.39Wamkazi wamangidwa ndi mmunake nyengo wakali wamoyo. Nampho ngati mmunake wakara wali huru kukwatiwa mndi waliyonche uyo siwamkonde, nampho pakati pa Ambuyepe. 40Nikali pakati pa malamulo yanga, siwakhale ndi chisangalalo kupunda ngati siwalame ngati umowali. Ndi niganiza kuti naneine nili ndi mzimu wa Mulungu.

Chapter 8

1Ndi chipano pakati pavakwaya vidachochedwa mayamiko kwa chosepha tijiwa kuti ife thaonche til ndi maarifa: maarifa kupeleka madama, ila chikondi chimanga. 2Ikakala munthu waliyenche waganizila kuti wajhiwa chinthu chakuti, unthu mmeneyo wakhali kujhiwa ngati umifunikiwa kujhiwa. 3Nampho ikakala mmoji wao wakhamkonda Mulungu, munthu mmeneyo siwajwike naye.4Ila kuhusu kudya vakudya ivovidachochedwa mayamiko kwa chosepha: tijhiwa kuti, "chosepha si chinthu katika jhiko lino," ndi pakuti palibe Mulungu nampho mmojhi pe. 5Pakuti aliambili athanidwa miungu ikakala kumwamba au pa jhik la panchi, ngati munjha vili vimungu ndi znya ambuye ambili. 6Ingakale kwanthu kuli ndi Mulungu mmoji ambae ni Ambuye. Vinthu vonche vachoka kwake, nafe tilama kwake ndi Ambuye mmoji Yesu Kristo, ambapo kwake vinthu vilipho, ndi kwaiye ife tilipho.7Hata chimwecho ujuzi palibe mkati mwa kila mmojipambuyo pake, ambili adashiriki ibada za chosepha yapa ale, ndi hata saachino akudya vakudya ivi ngati kuti chinthu chachochedwa mayamiko kwa chosepha, nchitho zao zawanangidwa pakuti ni mapungufu.8Nampho chakudya ife kwa Mulungu. Ife osati oipa sana ngati sitijh, wala abwino sana ikakala sitinjhe. 9Nampho mkhale makini pakuti uhuru wanu usidahala ndande yakuiphichana uyowali dhaifu kupitila imani. 10Hebu ganizila kuti muntu wakuona, iwe ulindi juhudi, ukudya chakudya katika hekalu la chosepha. Maganizo yake muntu uyu siwe ganizilidwa hata iye naye wadye vinthu vidachochedwa mayamikokwa chosepha.11Kwa chimwecho kwa chifuko ya ufahamu wako wa uzene pamwamba pa asili ya chothepha, kaka kapena dada wako wali ndi mapungufu, ambae nae Kristo wadafa kwa chifuko chake, siamwangamize. 12Chimwecho, yapouchintha dhambi dhidi ya kaka ndi dada zake ndi kujhipwentheka. 13Kwa chimwecho, ikhakala chakudya chisababisha kumkwaza kaka, kapena dada, sindidya nyama kamwe, ili sinidasababisha kaka kapena dada wanga kugwa.

Chapter 9

1Ine sinili oyangala inesinli otumika? Ine sinidamuone Mpulumusi? Anyiimwe simul vipacho va nchito yanga kwa Mpulumusi watu? 2Ikakala ine osati otumika kwa wina chabwino otumika kwa anyiimwe. Pakuti anyiimwe ndi chizindikilo cha utumii wanga kwa Mpulumusi.3Ichi ndo chojikambilila changa kwa anyiwaja anizuzumila ine. 4Bwanji tilibe haki ya kuja ndi kumwa? 5Tilije haki yotenga wamkazi uyo wakulubalila ngati umo achitila otumika wina, ndi achabale Ampulumusi ndi Kefa? 6Kapena ndiine neka ndi Barnaba kuti tifunika kuchita nchito?7Ndiyani wachita nchito ngati asilikali kwa mtengo wake mwene? Yani wavyala mtengo wa zabibu wasadaja matunda yake? Au yani wawesa wasidamwa likama lake? 8Bwanji nikamba yaya kwa malamulo ya umunthu? Lamulo nalo silikamba yaya?9Pakuti yalembedwa, palamulo la Musa, "siudaimanga ng'ombe pakosi yapo ikuja chakudya. mdizene kuti yapa Mulungu wazikokomeza ng'ombe?" 10Au simkamba yemeneyo kwa ndande yatu? Yalembedwa kwa ndande yatu, chifuko iye walimo chakudya ifunika kulima kokulupalila, ndi iye wavuna ifunika wavune koganizila akakala pamoji katika kuvuna. 11Ikakala tudavyala vinthu va muntima kati yatu, bwaji ndi mau la likulu kwatu tikavuna vinthu vammatupi kuchoka kwanu?12Ikakala wina adapata haki ii kuchoka kwanu bwanji ife osati kupunda? Ata chimwecho tidaipemphe haki ii. Pambuyo pake, tidakulupalila vinthu vonche kuona sikale cholakwicho cha mau la Mpulumusi. 13Simjiwa kuti onche achita nchito kukanisa apata chakudya chao kuchoka kukanisa? Simjiwa kuti onche achita nchito pa madhabahu apata pamalo ya chija chichocheda pa madhabahu? 14Kwa icho Mpulumusi wadatalika kuti onche alitangaza mau apate kulama ndi limene mau.15Nampho siwadaune vinthu vonche ivi ndi siwalemba yaya kuti chikale chalichonche chichitike kwa ndande yanga. Mbasa ine nife kuliko munthu waliyonche kuoneledwa kujielekela kwanga. 16Pakuti ngati nilalikila mau, nilibe ndande yojielekela.Pakuti nifunika kuchita chimwecho ndi ole wanga nisatalikila mau.17Pakuti nikachita ichi kwa kjichocha kwanga nili ndi mwawi nampho ikakala kwa kukonda kwanga nikali nili ndi nchito napachidwa kukala ojichocha. 18Basi pindu langa ni chiani? Kuti polalikilapo nilichocnhe mau popande mtengo ni bila kutumikila kwa uzene wa haki yanga nilinayo katika mau.19Atangati nakala ojisiilla kwa onche, nidali mbowa wa onche, dala kuti nikoze kwapata ambili sana. 20Kwa Wayahudi nidali ngati Myahudi, dala napate Wayahudi. Kwa anyiyao ali panchi pa lamulo, nidali ngati mmoji wa anyiyao ali panchi, pa lamulo dala napate anyiyao ali panchi pa lamulo nidachita chimwecho ine namwene sinidali panchi pa lamulo.21Kwa anyiwaja ali kubwalo kwa lamulo, nidali ngati mmoji wao kubwalo kwa lamulo, japo ine namwene sinidali kubwalo kwa lamulo la Mulungu, nampho panchi pa lamulo la Mpulumusi. Nidachita chimwecho dala napate anyiyao ali kubwalo kwa lamulo. 22Kwa amphawi nidli mphawi, dala napate ali mphawi. Nakala hali zonche kwa wanthu onche, dala kwa njila zonche nipate kwalamicha akumoji. 23Nane nichita vinthu vonche kwa ndande ya mau, dala nipate kukalapo katika mwawi.24Simjiwa kuti katika liwilo onche akoza atamanga liwito, nampho wadalandila chiko ni mmoji? Chapano tamangani liwito dala mpate chiko. 25Oyaluzidwa wajibana katika yonche yapo wakala pamayalzo. Achameneo achita chimwecho dala alandile chisoti cha ulemu cho wanangia nampho ife titawa dala tipate chisoti cha ulemu cha bwino. 26Kwa icho ine sinitawa bila ndande au nibula na nkhonyo ngati kubula pachabe. 27Nampho nilipweteka tupi langa ndikuchita ngati mbowa, dala kuti nikalalikila wina ine namwene nisakala okanidwa.

Chapter 10

1Ndifuna anyiimwe mjiwe kaka ndi kdada lango, kuti achate wanthu adali panchi pa mtambo ndi onche adapita pakati pa nyanja. 2Onche atabatiza ankale Amusa mkati mwa mtamba ndi pakati pa nyanja. 3Ndi onche dadya chakudya chichija cha mzimu. 4Onche adamwa cha kumwa chichija cha mzimu pakuti adamwela kuchoka pakati pa mtanda wa mzimu uo udachota , ndi mtanda uncha udali ndi Kristo.5Nampho Mulungu siwadakondoledwe sana ndi ambili wao, ndi maiti zao sidasambazidwa papululu. 6Ndipo vichito vomenevo vidali chifanizi kwatu, ili ife sitidakala wanthu onkumbila voipa ngati anyiiwo uma adachitila.7Msidankala oabudu, ngati winancho wao uma adali ii nde ngati umo idalembeledwa, "wanthu amakala panchi ndi adya ndi kumwa, ndi adaima ndi kuvina kwa kumbilo la chiwelewele" 8Tusidachita chigororo ngati ambii wao umo adachitila. Adafa siku limoji wanthu ishirini na tatu elfu kwa ndande imeneyo.9Wala itidamwesela Kristo ngati ambili wao umoadachitila ndi adawanangidwa ndi njoka. 10Nampho ncho msidanung'unika, ngati ambili wao umo adanung'ukila ndi kuwanangidwa ndi angelo wa kupha.11Basi vichito vimenevo vidachitika ngati ngati chifanizi kunthu yadalembedwa ili kutuanya ife taganizilidwa ndi kunta kwa mmayambilo. 12Chipano kila uyowajiona waima wa kale makinji wasidaja kugwa. 13Palibe oselo la kupatani ilo lili kawaida ya wanadamu ola Mulungu ndi mwaminifu. Siwakusiani mueseledwe kupilila kukoza kwanu pamoji ndi esela iye siwakuninkeni kama la chokelo, ili mukoze kuvumiliya.14Chipano, okondedwa wanga, intaweni ibada ya chosepa. 15Ndi kamba namwe ngati wanthu ali ndi njelu, ili mulamule pamwamba pa ilo ndikamba. 16Chikombe cha baraka tuchibaliki, osati kugwilizana ndi Kristo? Mkate uja tuumeza, osati kugwilizana ndi ntupi la Kristo? 17Pakuti mkate ndi umoji, ife tuli ambili tuli ntupi limoji, ife onche tulandila mkate umoji kwa pamoji.18Apenyeni wanthu aku Israeli: Bwa! Anyiwaja onche akudya dhabihu osati kugwilizana pakati pa mazabao? 19Ndikambe chiyani basi? Kuti chosepa ndi chinthu? Au kuti chakudya ocho chachochedwa nchembe chosepa ndi chinthu?20Nampho ndikamba pamwamba pa vinthu vija ivoachocha nchembe wnthu apagani pakuti achocha vinthu ivi kwa mizimu ndi osati kwa Mlungu. Nane sindifuna anyiimwe kugwilizana ndi mizimu! 21Simkoza kumwela chikombe cha Ambuye ndi chikombe cha mizimu. Simkoza kugwilizana pakati pa meza ya Ambuyendi pakati pa meza ya mizimu. 22Au tumtila mbuye nchonche? Tuli ndi mphavu zaidi yake?23"Vinthu vonche ndi halali," nampho osati vonche vifai. "Vinthu vonche ndi halali," Nampho osati vonche viwajenga wanthu. 24Palibe hata mmoji wadakafunafuna ya bwino yake pe. Badala yake, kila mmoji wadakafunafuna yabwino ya nchake.25Mkoza kudya kila chinthu chigulichidw kukosani bila kufunchila funchila ndande ya maganizo. 26Pakuti, "jiko ndi chuma cha Ambuye, ndi vonche vilija za." 27Ndi munthu uyosiwakhulupalila wakolalikani kudya, ndi mfuna kupita, idyani chalichonche ichosiwakuninkheni bila kufuncha maswali ya maganizo.28Nampho munthu wakakukambilani, "chakudya ichi chachoka ku nchembe ya wapagani." Msidadyali ii ndande yake uyowakukambilani, ndo ndande ya maganizo. 29Nane sindimaanisha maganizo yanu, ila maganiuzo ya yuja mwiancho. Pakuti ndande chiyani ufulu wanga uhukumidwe ndi maganizo ya munthu mwina? 30Ikakala ine nitumia chakudya kwa kuyamikila, ndande chiyani nitukanidwe kwa chinthu ambacho ndayamikila?31Chapano, chalichonche ichamkudya au kumwa, au chalichonche ichomuchita, chitani yonche ndande ya ufulu wa Mulungu. 32Msida akosesha Wayahudi wala Wasyunani, wala kanisa la Mulungu. 33Esani ngati ine umaniesela kuwakondecha wanthu onche kwa vinthu vonche. Sindifunafuna faida yanga namwene, ila ya mwina. Nane ndichita mchimwechi ili apate kulamichidwa.

Chapter 11

1Nichateni ine, ngati ine umondidamchatila Kristo. 2Chipano ndikuelekelani ndande umo mnikumbukilila pa nkhani zonche. Ndikuelekelani ndande mwagwila mwambo ngati umo ndida upeleka kwanu. 3Ndifuna mjiwe kuti Kristo ndi munthu wa wachimuna onche ndi wammuna ndi munthu wa wamkazi, ndi Mulungu nde munthu wa Kristo. 4Wammuna waliyonche waphempha kapena wali mneneri uku waviikila muthu wake wauchiticha manyazi muthu wake.5Nampho wamkazi uyo wapembphera kapena kuchocha uneneri uku muthu wake sindavinikilidwe wauchiticha manyazi muthu wake, chimozimozi ngati wametampala. 6Ngati wamkazi siwadaviniile munthu wake nde kuti chichi lake wasengelikale lalifupilifupi. Ngati iala manyazi wamkazi kusenga chichi kapena kumetedw basi wavinikile muthu wake.7Ndande sifunika wammuna kuvinikila muthu wake ndande iye nichifanizi cha ulemelelo wa Mulungu. Nampho wamkazi ndi ulemelelo wa Mulungu. 8Ndande wammuna wachokana ndi wamkazi. Nampho wamkazi wadachokana ndi wammuna.9Nampho wammuna siwadapangidwe kwa ndande ya wamkazi. Nampho wamkazi wadapangidwa ndande ya wammuna. 10Iyi nde ndande wamkazi wafunika kukala ndi langizo pamwamba pa munthu wake, kwa ndande ya angelo.11Ata chimwecho, mkati mwa Ambuye, wamkazi siwaliyoka popande wa mmua, kapena wammuna popande wamkazi. 12Mate ngati wamkazi wadachoka kwa wammuna chimwecho wammuna wadachoka kwa wamkazi ndi vinthu vonche vichoka kwa Mulungu.13Langani mwachinawene: bwnje ndizenu wamkazi wapempha Mulungu mutu wake ukale siudavinikilidwe? 14Bwanji atachiyambo choka sichidakuyaluzeni kuti wammuna wakaka ndi chichi lalitali ndi nchoni kwake? 15Bwanji chiyambo sichidakuyaluzeni kuti wamkazi wakakala ndi chichi lalitali ndi ulemelelo kwa iye? Mate yake wapachidwa lija chichi lalitali ngati chivalo chake. 16Ngati ikale munthu walienche wafuna kuchucha na pamwamba pa iyi, ife tilibe mtundu wina, kapena nyumba za Mulungu.17Mkati mwa utenga ukuja, ine sindikuelekelani, ndande yapmphezana, osati kwa pindu ikapanda ndi. 18Mate yake, ndevela kuti yapomphezana kunyumba ya mapemphelo, kuti kupatukana mwachinawene ndikuti kwa chipande ndikulupalila. 19Mate yake lazima ikalepo michucho mkatikati mwan, kuti yawo avomeledwa ajiwike kwa anyaimwe.20Mate yake yapomphezana, ichomkudya osati chakudya cha fumu. 21Yapomkudya kila mmoji wakudya chakudya chake mwene achanjake akaliosadye. Ata ngati uyu walindi njala, ndi uyu walojela. 22Bwanji palije nyumba zodyela ndikumwela? Bwanji mudelela nyumba ya Mulungu ndi kwachita mwano yao alije kanthu? Ndikambenji kwa anyaimwe? Ndikuelekeleni? Sindingate kukuelekelani pakati pa ili!23Ndande ndidalandia kuchokela kwa Ambuye chijha ndakuninkhani anyaimwe kuti Ambuye Yesu, usiku uja yapoadamuganamukila, wadatenga mkate. 24Wakate kuyamika wadautyola, "ili nde tupi langa, lilipo ndande yanu. Chitani chimwechi pakunikumbukila ine."25Chimwecho wakate kudya wadatenga chikome, ndi kukamba, chikombe ichi nde chizindikilo pa mwazi wanga. Chitani chimwechi kambili yapomkumwa, pakunikumbukia ine. 26Nyengo zonche yapomkudya nkate uwu ndi kuchimwela chikombe mkulengeza nyifa ya Ambuye mbakana yaposafike.27Kwaicho, uyo wakudya nkate kapena kuchimwela chikombecho cha Ambuye umosifunikila, siwapate milandu ya tupi ndi mwzi wa Ambuye. 28Munthu wajifunche mwene poyamba, ndipo waudye nkate, ndi kuchimwela chikombe. 29Mate kuti uyo wakudya ndi kumwa popande kujifuncha tupi lake, wakudya ndi kumwa chilango chake mwene. 30Hi nde ndande wanthu ambili mkatikati mwanu ndi odwala ndi dhaifu ndi anjanu wina amwalila.31Nampho tukajifuncha tachinawefe situlangidwa. 32Ila yapotulangidwa nda Ambuye, watubwelela, tusadajha kulangidwa pamojhi ndi jhiko.33Kwaichi, akuluwanga, nd alongowanga, yapo mpzana kufuna kudya, lindililanani. 34Munthu wakakala ndi njala, wadye kukomo lake, kuti yaposimphezane pasakalapo chilango. Nkhani zina izo mwalemba, sindikambileni yaposindifike.

Chapter 12

1Kupitila mbaso za mtima, kaka ndi dada zanga sindifuna mulepele kujiwa. 2Mujiwa yakuti yapo mudali osasali muda chogozedwa kuchata sanamu izosizimakambe, pajila zilizonje izo mmapelekedwa nazo. 3Ndiposo ndifuna mujiwe palibe walinje wakamba kwa Roho ya Mulungu wakakamba, "Yesu waningidwa lahana palibe waliese siwakambe, Yesu ndi Ambuye. Ingakale kuti kwa Roho Yoela.4Basi kui mboso yosiana yosiana, pakuti Roho ndi iye yuja. 5Ndi kuli kulangidwa kosiyana siyana, ndiposo Mulungu ndi iye yuja. 6Ndi kuli njito zosiana siyana, nambo Mulungu ndi iye yuja wazichita njito zonje pakati paonje.7Ndipo kila mmoji waningidwa kujiwa pakati pa Roho pafaida yake. 8Pakuti mundu mmoji waningidwa ndi Roho mau la ulemu, ndi mwina mau la zelu kwa Roho yuyuja.9Ndimwina wanikh kulimbika kwa roho iye yuja, ndi kwamwina kuchiticha ko lamicha kwa Roho imoji. 10Ndi kwamwina njito za mbavu, ndi mwina ulosi ndi kwamwina kukoza ndi kujiwa Roho. Mwina vindhu vosiyana siyana za mau, ndimwina kutafsili mau. 11Nambo Loho yuyuja wachita njito zoje, kuninga kila mundu mbavu pachisanga chake mwene.12Pakuti ngati vija tupi ndilimoji, nao uli ndi visemba vambili ndi visemba voje ndi vatupi lilija, chocho ndi Kristo. 13Pakuti pakati pa Loho mmoji taoje tidabatizida kukala tupi limoji kuti tili Wayahudi kapena Ayunani, kuti tili otumidwa au huru, ndi taonje tidamwechedwa Loho imoji.14Pakuti tupi opande misemba chimoji ila vambili. 15Ngakale mwendo sukambe, "pakuti ine opande janja, ine opande mmoji watupi," imeneyo siichita mmalo mwa tupi. 16Ndi ngakale kutu silikambe, "pakuti ine opande diso, ine ndi mmalo mwatupi," limene silichita kuti nde opande mmalo mwa tupi. 17Ngati tupilonje silikale diso, kudakala kuti kuvela? Ngati tupilonje lidakakala munthu, kudakakala kuti kununja?18Nambo Mulungu wadaia kila msemba watupi mmalo mwake ngati umowadakonjela mwene. 19Ndi ngati vonje vidakakala msemba umoji, tupi lidakakala pati? 20Chocho misemba yambili, tupi ndilemoji.21Diso sitikoza kulikambila janja, "niibe njito ndiiwe! ndipo mtu sukoza kuikambila ywendo, nilibe njito namwe." 22Nambo misemba yatupi vionekana kuti vili ndi ulemu pango'no vifuna kupunda. 23Ndi misemba yatupu tikhani za kutivili ndi ulemu pang'ono, tivinikha ulemu kupunda, ndi misemba yonje vilibe mvuto ndivokwada kupunda. 24Ndi chopana misemba yonje vili ndi mvuto vilibe afa yoningidwa ulemu, pakuti tayale vilemekezeda, nambo Mulungu wavitumikiza misemba vonje pamoji ndi wavinikiga ulemu kuposa ivo vilemekezedwa.25Wadachita chimwecho kuti sipadakala ndi kugawanyika kupitila tupi, kuti misemba yonje vituzane kwa chikondi cha pamoji. 26Ndipo msemba umoji ukapwtekedwa misemba yoye ipwetekedwa kwa mpamoji pena ndawi msemba omoji ukalekezedwa, msemba yonje ikondwele kwa mpamoji. 27Chopano anyiimwe ndi tupi la Kristo, ndi misemba kila chimoji pachoka.28Ndi Mulungu waika mkanisa kui opuzila chakawile alosi, chakatatu apuzisi, ndioiso waja onje achita vindu vavikulu ndipo njitozochitisa, waja atangatilao, anyiiwo achita njito yochogoza, ndioje ali ndi mikambo yosiana yamau. 29Bwa ife onje ndi otumidwa? Ife onje ndi alosi? Bwife onje tichita njito yochitisa?30Bwa ife taonje tilimbavu yolamicha? Ife onje tikamba kwa mau? Ife onje tikambilila mau? 31Funa funani mbavu zilizakikulu, nane sinikulangizeni njila ili yabwino kupunda.

Chapter 13

1Tikambe kuti ndikamba kwa mau ya chimwatu ndi za angelo. Nampo ngati ndilije chikondi ndi kala chichulo hilila kapena maswela yopitilila. 2Ndikuti ndili ndi mwawiolengedwa ndi kjiwa kwazene kwajibisa ndi vichito vabwino ndikuti ndili chikurupalilo cho chosa mapiri. Nampho ikakala ndilije chikondi ine sikantu. 3Ndi tikambe kuti sindichoche kalikoche ndilinako ndikuadyecha apawi ndikuti sindilichoche tupi langa dala ndiochedwe moto, nampho ngati ndilije chikondi ine sindili kantu.4Chikondi ku kurupalilana ndi kutandizana chikondi siujikweza ndi kujichita chilibe mbwinya. 5Kapena ndeo siufuna nkani zake siupenya kuipichidwa msanga siuwelenga kuipa. 6Siukondwela voipa pambuyo pake kusangalalila pakati pauzene. 7Chikondi chidikamila kalikonche kukurupalila, chilindi mpavu pakati chili ndi kudikamila nkati zoche.8Chikondi sichikunta ikakara kulindiorota wonche siupite ikakara kulimkambo siute ngati sikukale mtundu wabwino siupite. 9Pakuti tijiwa malo yochepa tichifa yorote. 10Nampo ikakala iliya chichimichimi, ija uje chichimichimi siipite.11Yapo ndidali mwana, ndindakamba ngati mwana ndidaganiza ngati mwana ndidalamula ngati mwana, yapo ndidali wamuru ndida ya ika pampepete nkani za chibwana. 12Pakuti chapano tipenya ngati grasi ngati mpumu kumdima nampo ntawi ija tipenya na maso kwa maso chapano ndijowa ngati malo yochepa nampo ntawi ija sindi zindikile kupunda ngati ine ume ndidajiwikila kupunda. 13Nampo chipano nkani izi zitatu. Yalipo kupunda chikurupalilo ndikurupalilo likuja, ndichi kundi, nampo lilindi mate kupunda yaya ndi chikondi.

Chapter 14

1Chifuneni chikondi ndi kuumbila kupunda njito za mtima kupindichicha mkose kuchocha zolosa. 2Mate iye wanena kwa mikambo siwanena ndi wanhu ikapanda wakamba ndi Mulungu. Mate popande wazindikila kwa chifuko wanena vochitika vobisika pa mzimu. 3Nampho iye wachocha kulosa,wakamba ndi wandhu ndi kuwamanga, kuwatila mtima, ndi kuwatondoza. 4Iye wanena kwa mkambo wajimanga mwene, nampho iye wachocha kulosa walimanga kanisa.5Chipano nikumbila kuti anyiimwe mwa wonche mambe kwa mkambo, nampho kupunda ya yameneyo, nikumbila yakuti mchoche volosa. Uyo wachocha volosa ndi wamkulu kupunda iye wanena kwa mikambo (kapena wakelepo ndiwa kulongosola) Kuti kauisa lipeze kumangidwa. 6Nampho chipano akuluwanga ndi achalongo wanga, nikajha kwanu ndi knena kwa mikambo sinikutangatileni chiyani anyiimwe? Sinikza ikapanda ndikamba ndi anyiimwe kwa njila ya kujivumikula, kapena kwa njila ya njelu kapena ulosi, kapena kwa njila ya yaluzo.7Ikakala vindhu vosati ndi umoyo ngati filimbi kapena chinubi ngati voachoche sauti za mtundu sijhutikane bwanji, ndi chindhu chiti chivina? 8Kwa mate ikakala mbetete siichoche sauti yosajhiwike, ni mtundu uti mundhu siwajhiwe ya kuti ntawi ya kujhiika kwa nghondo? 9Mmwemo kwa anyiimwe. Mkachocha kwa lilime mau osati lene, ndi kwa mtundu wanji mundhu siwaelewe mchikamba? Simkale ndi mkamba palibe wakukuelewani.10Palibe, mashaka kuti kuti nimikambo ya mbili mtundu mtundu panjiko ndi palibe ata limojhi lopande mate. 11Nampho ikakala simjhiwa mate ya mikambo, sinikale mtendo kwa iye wanena, ndi iye wanena siwakale mlendo kwa ine.12Mmwemo ndi anyiimwe. Pakuti mkumbila kupunda kuona uzene wa Mzimu funani kuti mpunde kupunda kulimanga kanisa. 13Mmwemo iye wanena kwa miambo wapembhe wapachidwe kulongosola. 14Kwa mate ikapembha kwa mikambo Mzimu wanga, upembha, nampho njelu zanga zilibe vipacho.15Nichite bwanji? sinipembhe kwa mzimu wanga, namphoncho sinipembhe kwa njelu zanga. Sinikimbe kwa mzimu wanga, ndi siniimbe kwa njelu zanga nazo. 16Venavake, ukamkuzika Mulngu kwa mzimu, iye wali mlendo siwatanike bwanji "Amina." Yapouchocha mayamiko, ikakala siwajhia uchikamba?17Mate ni zene iwe uyamikia bwino, nampho yujha mwina siwamangidwa. 18Nimuyamikila Mulungu pakuti wanena kwa mikambo kupunda anyiimwe mwaonche. 19Nampho pa kanisa ndi heri ni nene mau ya sano kwa kujhijhiwa kwanga kuti nipeze kukuyaluzani wena, kupunda ya kunena mau kumi elfuya mikambo.20Akuluwanga ndi achalongowanga, msadakala wana pa kuganizila panu. Pambuyo pake kukihotana ndi yoyipa, mkale ngati wana ateta. Nampho pa kuganiza panu mkakale wandhu wakuluakulu. 21Yalembedwa pa matauko, "Kwa wandhu amikambo yena ndi kwa milomo ya alendo sininene ndiwandhu anyiyawa. Wala ata chimwech siani vela," wanena Ambuye.22Mmwemo, ndini ni vizindikilo, osati kwa okulupalile. Ikiwa kwa osakulupalile, nampho kuchocha kulosa ndi vizindikilo, osati kwa osakulupalile. 23Haya ikakala kanisa lonche lasoghanika pamojhi ndi wonche akambe kwa mikambo, ndi wena osakulupalile alowa, bwanji siakoza kunena kuti muli ndi viuta?24Nampho ikakala wonche mchocha oosi ndi osakulupalile kapena mlendo wakalowa, siwachawishidwe ndi yonche waavela. Siwalamulidwe ndi yonche yakambidwa. 25Vachisiri cha mtima wa iye yavunukulidwa. Yochekela yake, wadkagwa chamimba ndi kumlambila Mulungu. Wadakavomela kuti Mulungu wali pakati panu.26Chiyani chichatala basi, kaka ndi achidada wanga? Yapomphezana pamojhi kila mmojhi wali ndi Zaburi mayaluzo, kumasuka mimambo kapena, kutandauza, chitani kila chindhu kuti mmange kanisa. 27Ngati waliyenche wanena kwa mikambo, akalapo awili kapena atatu, ndi kila mmojhi pa zamu ndi wandhu lazima kutandauza ichochanenedwa. 28Nampho ngati popande mundhu wa kutandauza basi kia mmojhi wa anyiiwo wakale chete mkati mwa kanisa. Mmwemo kila mmojhiwakambe yeka ndi kwa Mulungu.29Ndi olosa awili kapena atatu ojhumbala, ndi wena avechele kwa kukambilila ichochanenedwa. 30Nampho uyowakela wakavunukulidwa kandhu pa utumi yujha uyo wadali mkunena wakale chete.31Pakuti kila mmojhi wanyiimwe wakoza wakoza kuchocha olosi mmojhi pambuyo pa mwena kuti kila mmojhi wakoze kujiyaluza ndi wonche akoze kutilidwa mtima. 32Pakuti mizimu ya olosa yali panchi pa kupanyeleledwa ndi olosa. 33Pakuti Mulungu osati Mulungu wa nchondo, akapande wa mtendele. Ngati umoili pa makanisa yonche ya34Ikufunani wachikazi mkale chete pa kanisa. Pakuti simdalamulidwe kukamba. Pambuyo pake mfunika kukala ojhichicha, ngati mmwemo matauko umoyakambila. 35Ngati kuli chalichonche akumbila kujhiyaluza, basi awafunche achamnao mmakomo. Pakuti ndi nchoni kwa wamkazi kukamba pa kanisa. 36Bwanji mau la Mulungu lidachoka kwanu? Bwanji lakufikilani anyiimwe pe?37Ngati mundhu wajhiona kuti ndi olosa kapena wa mumtima, wafunika yoayajhiwe yochitika ndiwalembela ya kuti ndi yotumidwa ndi Ambuye. 38Nampho ngatiosa yajhiwe yaya, msiyeni wasadajhiwikana.39Mmwemo basi, kaka ndi achidada wanga, funani kupunda kchocha olosi, ndi msadamchekeleza mundhu waliyenche kunena kwa mikambo. 40Nampho vochitika vonche vichitike kwa ubwino ndi kwa kusamalalila.

Chapter 15

1Chipano nikukumbuchani anya chimwene ndi anyachemwali, kukuza utenga nidakulelikilani, umene mdaulandila ndi kuima nao. 2Ndi mu utenga uu mdapulumuchidwa , ngati mkaligwila chigwilile mau nidakulalikilani anyiimwe , ingakale mdakulupilila osati chaje.3Mate yake nidakuchochelani vija nidavilandila namwene chiyambile kale kuti Kristo wadafa chifukwa cha madumo yatu ngati malembo umo yanenela. 4Ngati umo yali malembo kuti wadazikidwa ndi siku la katatu wadahyuka.5Ndi kuti wadamcvhokela Kefa, kenaka anyiwaja kumi ndi awili. 6Kenaka wadachokela wina mia tano pamoji mwa anyameneo ambili akali amoyo akumoji atokufa. 7Pambuyo wadamchokela Yakobo ndi otumidwa onche.8Potela kwa wanthu onche wadanichokela ine ngati munthu uyo wabadwa nthawi yake siidakwanile. 9Ine ndi munthu wa mng'ono pakati pa otumidwa, sinienela kutanidwa otumidwa, ndande nidalivuticha kanisa la Mulungu.10Nampho kwa lisungu la Mulungu nili ngati umonili ndi lisungu lake kwanga silidali chaje, pambuyo pake nidalimbikila osati ngati onche, nampho siidali. Ine koa lisungu la Mulungu lili mkati mwanga. 11Kwa icho ngati ine kapena anyiiwo, tilalika chimwecho ndi tikulupilile chimwecho.12Ngati Kristo wadalalikidwa ngati uyo wadahyuka kwa akufa, ikala bwanji akumoji wanu akamba palije chi hyukililo? 13Nampho ngati palibe chihyukililo cha akufa koma Kristo naye siwadahyuke. 14Ndi ngati Kristo siwadahyuke, ulaliki watu ni chaje ndi chikulupi chatu ni chaje.15Ndi tapezekana kukala mboni wa unami kumkuza Mulungu, ndande tidamchitila mboni Mulungu kuti wadamyucha Kristo, nyeno siwadamhyuche. 16Mate yake ikakala zene kuti akufa saa hyuka Kristo naye siwadahyuke. 17Ndi ngati Kristo siwadahyuchidwe, chikulupi chanu ndi chaje ndi mkali mmachimo yanu.18Kwa icho ingakale aniwaja afa mu jina la Kristo saakale atosowa. 19Ikakala kwa moyo uu okawachapano nde Chikale chikulupi chatu, ife siikale ndi wanthu odandaulidwa osati ngati wanthu onche.20Nampho chapano Kristo wahyuka kuchoka kwa akufa ayamba kwa akufa. 21Ngati umo ili nyifa yabwela pajiko la panchi kupitila munthu mmoji, koma kuhyuchidwa nako kwabwela kupitila munthu mmoji.22Chifukwa ngati mwa Adamu wanthu onche akufa ndi kupitila Kristo onche achitidwa moyo. 23Nampho kila mmoji mu mtundu wake: Kristo poyamba pambuyo anyiwaja ali mkati mwa Kristo nyengo yobwela kwake.24Nde simkale msitizo, paja Kristo yaposiwapeleke ufumu kwa Mulungu, pamene yapo siwakauliche malamulo, ndi mphavu zonche. 25Mate, Kristo wakala fumu, mbaka Mulungu yapo siwaaike adani wake panchi pa myendo yake. 26MdaniMdani otela kuwanangidwa ndi nyifa.27Pakuti waika kila chinthu, panchi pake, siimkuza Mulungu ndande iye nde uyo waviika vinthu vonche panchi pa Kristo. 28Nampho yapo vinthu vonche yapo sivikale panchi pa ufumu wa Kristo, pamene Kristo naye siwajiike panchi pa Mulungu wadaika vinthu vonche panchi pa ufumu waiye, kuti Mulungu wakale pamwamba pa vinthu vonche.29Ngati kulibe kuhyuchidwa, wanthu waja abatiza ndande ya akufa akulupilila chiyani ngati akufa sahyuchida bwanji kubatiza ndande yao? 30Ndi ife ndande chiyani kujiika?31Anyachimwene ndi anyachemwali wanga, kupitila kujielekela kwanga mwanyiimwe kuli mwa Kristo Yesu Ambuye watu, nikamba chimwe nikufa kila siku. 32Inipundulila chiyani mmapenyelo ya wanthu. Ngati ni uabulana ndi vinyama vong'ang'ala ku Efeso, ngati akufa sahyuchidwa? Leka tidye ndi kumwa, pokala mawa tikufa.33Msanyengedwa, ubwenji oipa uwanga ukalo wabwino. 34Ukani! Muyambe ukalo wa malinga, msaendekela kuchita machimo, ndande akumjiwa Mulungu, nikukamilani imene ndi nchoni yaikulu kwanu.35Nampho munthu wakoza kufuncha wakufa siwahyuchidwe bwanji, siwakale ndi tupi la mtundu bwanji. 36Yamene ndi mafuncho yopande mate, ukavyala mbegu ngati siifa huti siipuka.37Icho uvyala ndi mbeu pe ikale ya ngano kapena injake iliyonche, osati mtengo wa mphumphu uwo siumele. 38Mulungu waipache mbeu tupi ilo walifuna iye mwene, kila mbeu ipata tupi lake la yoka. 39Matupi ya volengedwa vonche si ifanana matupi ya wandhu ndi ya mtundu Umoji ya vuinyama ndi ya mtundu wina ya mbalame ndi ya mtundu wina ndi matupi ya nchomba nayo ya mtundu unjake.40Kuti matupi ya kumwamba ndi matupi ya jiko la panchi ubwino wa matupi ya kumwamba ni unjake ndi ubwino wa matupi ya jiko la panchi ndi unjake. 41Kuli ubwino wa jua, wa wezi, ndi wanthondwa ingakale nthondwa ubwino wake zimasiana.42Chimwecho nde umo ili chihyuchido cha akufa tup lizikidwa lowanangika lihyuchidwa la bwino. 43Livyalidwa munchoni, lihyuchidwa mu ubwino livyalidwa mopande mphavu, lihyuchidwa mu mphavu. Livyalidwa tupi la chiyambo, lihyuchidwa mu mphavu. 44Livyalidwa tupi la chiyambo, lihyuchidwa tupi la mzimu, ikakala lilipo tupi chiyamb ndi la mzimu lilipo.45Nde malengo umo yalembedwa, munthu oyamba Adamu wadakala mzimu uli moyo Adamu otela ndi mzimu ohyuchicha. 46Nampho wa mzimu siuchogolela, koma uja wa chiyambo kenaka uja wa mzimu .47Adamu oyamba wadalengedwa kwa doti, munthu wa kawili wadachokela kumwamba. 48Ngati umo wali wadalengedwa kwa doti nde umo ali ajhiko la panchi, anyiawo ali akumwamba ali ngati uyo wachokela kumwamba. 49Ndi ngati umo tatengela mphumi yake yuja wadoti nde umo sititengele mphumi yake iye wa kumwamba.50Achiabale wanga icho nikamba ndi kuti nyama ndi mwazi sivikoza kusiilidwa ufumu wa kumwamba, ingakale kuwanangika kusiilidwa kosa wanangike. 51Penyani, nikukambilani, chisisi sitigona taonche nampho tanche siting'anamuka.52Kwa dakika imoji, kutimila ndi kupanula, nyengo ya mbetete yotela, pakuti mbetete siilile ndi akufa sahychidwe, asadaka ndi kuwanangika nafe siting'anamuka. 53Pakuti lowanangika livale losawanangika ndi la kufa livale losafa.54Nampho awanangika ukava osawanangike ndi wakufa ukala osafe, nde yapo siuje mkambo walembedwa nyifa yamezedwa mu kuwina. 55Nyifa, kuwina kwaku kulikuti? Kupweteka kwako kulipati?56Kupweteka kwa nyifa ndi machimo, ndi mphavu ya machimo ndi tauko. 57Nampho tumyamike Mulungu watipacha kuwina kupitila Ambuye watu Yesu Kristo.58Kwa icho okondedwa,nyachimwenendanyachemwali wanga, limbani msatingizika nthawi zonche chitani nchito ya Ambuye, ndande mjiwa nchito yanu kwa Ambuye osati ya chaje.

Chapter 16

1Chipano pa zotandizira a Kristo, ngati umo ndiakambila Kugalatia chimwecho mfunika kuchita. 2Pasiku loyamba la sabata, waliyonche wajipatulapo kanthu ndi kusunga, ngati umo mkozela. Chitani chimnwechi kuti kusakhalapo sonkho nyengo ndi kabwelancho.3Yapo sindifike, waliyoncho uyo simumsankhe, sindimphache ndi karata pamojhi kupeleka nchembe zanu Kuyerusalemu. 4Ndi ngati bwino ndi ine kupita, sapite pamojhi ndi ine.5Nampho sindifike kwanu, yapo sindipitile ku Makedonia. Pakuti, sindipitile Kumakedonia. 6Kapina ndikhoza kukhala namwe, kapena kutkanyengo yonche yozizila, kuti mkoze kunditandiza ulendo wanga paliponche yaposindipite.7Pakuti sindikulupilia kukuonani pafupi yapa, ndikulupalila kukhala namwe panthawi ya kuti ngati Ambuye akandiloleza. 8Nampho sindikale ku Efeso mbaka na ku Pentekoste. 9Pakuti chicheko chamasuka chifukwa chaine, ndikuli adani ambili anichucha ine.10Chipano Timotheo wakaja, muoneni kuti wali lmoji ndi anyaimwe samuope, wachita nchito ya ambuye ngati umomchitila. 11Munthu waliyonche wasamyoze mutandizane nae mwa mtendele, kuti wakoze kundifikira ine. Ndimkulupalla wajhe pamojhi ndi mabale. 12Chipano mbale wathu apoolo, ndidamtila mtima kupunda pa kumuendela anyaimwe pamojhi ndi mabale. Nampho chipano siwadafune kujha. Ata chiwecho siwaje wakakala ndi nyengo.13Kalani maso, imani nganganga, mchite ngati wachimuna, mkhale ndi mphamvu. 14Chitani yonche mkati mwa chikondi.15Mlijiwa banja la Stefana. Mjiwa kuti adali okulupalila oyamba ku Akaya, ndikuti adajiika achinawene kutumikila Akristo. Chipano ndi kuphemphano akuu wanga ndi mwahalonga wanga. 16Kalani ovela kwa wanthu ngati anyameneo ndi waliyonche uyo watandiza nchito za ochita nchito pamoji ndi ife.17Ndikondwa pofika Stefana, Fotunato ndi Akiko. Aima pamalo yapo mmafunika kukalapo. 18Pakuti akondwecha mtima wanga ndi mitima yanu.Kwaicho chipano ajiweni wanthu ngati anyiyawa.19anthu akuasiya apeleka oni kwayaiwe. Akila ndi Priska akulonjelani mzina la Ambuye, pamojhi ndi ampingo akumiji yao. 20Achaabale anga onche akulonjelani lonjelani mwa chikondi chenicheni.21Mimi, Paulo ndilemba izipa jha langa. 22Waliyonche ngati siwakonda Ambuye, akale wotembereredwa, Ambuye majani. 23Ambuye Yesu akudaliseni. 24Chikondi cha Mulungu chikale namwe mkati mwa Kristo Yesu.

2 Corinthians

Chapter 1

1Paulo otumidwa wa Kristo Yesu kwa ukondwelelo wa Mulungu, ndi Timotheo m'bale wathu, kwa kanisala Mulungu lili Kukorintho ndi okulupilila onche ali kuchigao chonche cha ku Akaya. 2Mwai ukale ndi mtendele kuchoka kwa Mulungu atate watu ndi Ambuye Yesu Kristo.3Ndi aelekedwe Mulungu, ndi atate wa Ambuye Yesu Kristo iye ndi atate olekelela ndi Mulungu wa chilondozo chonche. 4Mlungu watitondoza mmavoto yatu yonche kuti tikoze kuatondoza yao ali mmavuto.5Pakuti ngati umo yapundila mavuto ya Kristo mkati mwatu nde umo tipundila kutondozedwa ndi iye. 6Ikakala tipata mavuto ndi ndande ya chitondozo ndi chipulumuso chanu. Tikatondozeka ndi ndande yakutondozani anyiimwe ndi kukugwilani janja janja mpate mphavu yoima chiimile mavuto yamweyaja tivutika ife. 7Chikulupi tilinacho ndande yanu ndi chiimile, tijiwa kuti mkazwilizana ndiife mmavuto yatu, simgwilizane ndiife mutondozo latu.8Pakuti sitifuna, msajiwa nkhari ya mavuto yajatipeza ku Asia, kuti tidalemezedwa osati ngati mphavu zatu mbaka tidadula chiulupi. 9Tidali ngati yao alangidwa nyifa kuti muyaluzidwe kumkulupilila Mulungu, wadahycha akufa, pamalo pokulupilila mphavu zatu tawefe. 10Iye wadeatipulumucha mu nyifa ndi waendekela kuti pulumucha, ndi taika chikulupi kuti siwatipulu muchecho.11Siwachite chimwechi ngati umo mtitangatila kwa mapemphelo yanu. Kwa icho ambili saachoche mayamiko pamalo patu, ndande ya chikondwelelo cha mwai tidapachidwa kupitila mapemphelo ya ambili.12Ife tiidamila chinthu chimoji, kuti takala pajiko la panchi pakati panu kojichicha ndi ukalo wa bwino tapachidwa ndi Mulungu, sitidachogozedwa ndi malango ya wanthu nampho kwa mwai wa Mulungu. 13Tikulembelani vinthu ivo mkoza kusoma ndi kuvana navo ndikulupilila kuti simvane navo bwino. 14Mate mbaka chapano mwavana nane pang'ono tijiwa kuti pa siku la Ambuye Yesu, simkoze kjidama ndande yaife ngati umotijilama ife ndande yanu.15Ndande iyi nidali ndi mphavu kukuza ichi, nimafuna kuja kwanu poyamba, kuti mkoze kulandila pindu loendeledwa mara kawili. 16Nimafuna kukuendelani nyengo nipita Kumakedonia. Kenaka nimafuna kukuendelanincho nyengo yobwela kchoka ku MAkedonia, ndi anyiimwe kunituma ine nyengo nipita Kuyuda.17Yapo nimaganiza mtundu uu, bwa nimakaikilakaikila? Mganiza nichita vinthu kwa maganizo ya wanthu kuti nikamba yetu ndi iyayi nthawi imweyo. 18Nampho ngati Mulungu umo wali okulupilika, sitikamba vonche "yetu" ndi "iyayi."19Pakuti mwana wa Mulungu Yesu Kristo, mmene Silvano, Timotheo, ndi ine timamlalikila siwadali munthu wa "yetu" ndi "iyayi" nampho nyengo zonche iye ndi "yetu." 20Pakuti lonjezo la Mulungu ni "yetu" kwa icho kupitila iye tikamba, "Amina," kwa kuyera kwa Mulungu.21Chapano, ndi Mulungu watiimika chiimile ife ndi anyiimwe mwa Kristo ndi iye nde watituma. 22Iye nde wadatiika chidindo tikale wanthu wke ndi kutiikila mzimu mmitima yatu ngati chogwilila vinthu vimene taikilidwa.23Pambuyo pake nimpemphe Mulungu kunilalikila ine kuti ndande idanichita nisadaja ku Korintho ni kuti nisadakulemelelai. 24Osati tichogolelo chikulupi chanu kwa mphavu nampho tili limoji pa chimwemwe chanu, ndande pa chuikhulupi chanu muima chiimile.

Chapter 2

1Kwa icho nidalamula kwa malo yanga namwene kuti sinidakajancho kwanu katika hali ya kudandaula. 2Ngati nidakusababishiani aniimwe kupwetekeka ni yani wadakani kundwecha ine, nampho ni yuja wadapwetekeka ni ine?3Nidalemba ngati umo nidachitila dala kuti muda sinije kwanu nisakoza kupwetekeka ni waja ambao adakachita anichite nisekelele. Nilinao ujasili kuhusu anyiimwe mwaonche kuti kukondwa kwanga ni kukondwa kumkuya muli nako anyiimwe mwaonche. 4Pakuti nidakulembelani anyiimwe kuchokana ni mazunjo yakulu, ni vuto la mitima, ni kwa misozi yambili, sinidafune kukusababishiani anyiimwe kupwetekeka. Badala yake nidafuna mjiwe chikondi cha chikulu nilinacho chifukwa chanu.5Ngati kuli waliyonche wasababisha kupwetekeka wadasababishe tu kwa ine, nampho kwa mtundu fulani, bila kuika ukali wa ukulu - kwanu anyiimwe mwaonche. 6Ii azabu ya munthu mmeneyo kwa ambili ikwana. 7Kwa icho chapano badala ya azabu, mfunika kwalekelela ni kwatondoza. Chitani chimwechi dala kuti wasakoza kulepela n dandaulo yopunda.8Kwa icho nikutilani mtima kupenyelela chikondi chanu padanga chifukwa chanu. 9Ii nde ndande nidalemba, dala kuti nikoza kuesani ni kujiwa kuti ngati ni aulemu katika kila chinthu.10Ngati mumulekelele waliyonchye, nanencho pia nimlekelela munthu mmeneyo. Chija nachilekelela ngati nalekekela chalichonche chalekeleledwa kwa pindu lanu katika kukalapo kwa Mpulumusi. 11Ichi ni kuti satana wasafika kutuchitila vonyenga. Pakuti ife osati owelela kwa mipango yake.12Chicheko chidecha kulidwa kwanga ni Ambuye yaponidaja kwanu muji wa Troa paja. 13Ata chimwecho, nidalije mtendele wa mtima, kwandande sinidamtume m'bale wanga Tito paja. Chimwecho nidasiya ni nidabwela Kumakedonia.14Nampho wayamikidwe Mulungu, ambae katika Mpulumusi muda wonche watuchogoza ife katika kukoza. Kupitila ife wasambaza mnunkho wa bwino ya kjiwa kwake pamalo ponche. 15Pakuti ife kwa Mulungu ni mnunkho wa bwino wa Mpulumusi, onche kati ya anyiwaja apata ombolelo, ni mnunkho ni kati ya anyiwaja apwetekeka.16Kwa wanthu ambao apwetekeka, ni manukato kuchoka nyifa mpaka nyifa. Kwa anyiwaja apataombolelo, ni mnunkho wa bwino kuchoka kulama mpaka kulama. Ni yani wafunika vinthu ivi? 17Pakuti ife osati ngati wanthu ambili agulicha mau la Mulungu kwa pindu. Badala yake, kwa kukadwa kwa kukonda, tikamba katika Mpulumusi, ngati muja titumidwa kuchoka kwa Mulungu pamaso pa Mulungu.

Chapter 3

1Bwa tayamba kujikuza tawene njo? Sitifuna kalata ya kupendekezedwa kwanu pena kuchoka kwanu, ngati baadhi ya wandu wa tifuna? 2Anyiimwe mawene nikalata yatu yokondedwa, iyo idalembedwa mutima mwatu, iyoijiwikana ndi kusomedwa ndi wandun onche. 3Mulangiza kuti anyiimwe ndi kalata kuchoka kwa Kristo, iyoitachochedwa ndi ife. Idalembedwa opande kwa wino bali kwa loho ya Mulunu uyo wali hai. Sidalembedwe pamwamba pawale ndipo pamwamba pa vibao yamitima wawandu.4Ndiu ndo kujituma uwotili nao pakati pa Mulungu kupitila Kristo. 5Sitiji kulupilila tawefe kodai chilichonje ngati kuchoka kwatu. Pambuyo pake, kujikulupilila kwatu kuchoka kwa Mulungu. 6Ni Mulungu wali wadatichita tikoze kuala otumidwa wa agano la chopano. Ili akgano opande za kalata bali ndi la loho. Pakuti kalata ikupa, nambo loho ichoka kupuma.7Chopano njito ya nyifa iyoidli yasepedwa pamalembo pamwamba paywala idali pandande ya kukulupilila kuti wandu Aiziraeli sadapenye moja kwa mojua pamaso pa Musa. Iyi ndi pandande yaufulu wa pamaso pake ufulu uwo udali umafifia. 8Bwa, njito ya Roho sikala ndi ubwino kuposa?9Pakuti ngati njito yolangidwa idal ndi mtendele, ndi mala kangati kupunda njito ya uzene izidi sana pa mtendele! 11Ndi uzene kuti chifa chidachitidwa mtendele kuti chilibe mtendele njo patai paulemu uu, pandande ya mtendele uposa. 10Pakuti ngati chifa chidali ndichipita chitali ndi mtendele, ndi kwa kiasi chanji kuposa chifa chidali cho lamasichikale ndi mtendele!12Pakuti tijikulupilila chocho, tilindi ujasili kupunda. 13Sitili ngati Musa, uyo wadaika ulemelelo pamwamba pamaso pake, ili kuti wandu Aisraeli sadakoza kuupenya moja kwa moja pamatelo pa mtendele uwo udali ndiusowa.14Nambo kjiwa kwao kudali kwamangidwa. Ata ngati siku ili kufuna akunvuja kukali ukala pamwamba payao asoma wa agano la kale. Sidaikidwe wazi, pandande ndi pa Kristo yoka wachochedwa patali. 15Nambo ata lelo, ndawi yalionje Musa yapowasomedwa, utaji wakala pamwamba pa mitima yao. 16Nambo mundu yapowanganamuka pa Ambuye, utaji uchochedwa.17Chopano Ambuye ndi Roho, pali ndi Roho ya Ambuye pali ndi mwanga. 18Chopano ife onje, pamoji ndi ngope zilibe sizidaikidwe utaji, zipenya mtendele wa mbuye. Tusindidwa mati mwa maonekedwe uuja wa mtendele kuchoka pa shada limoji la mtendele kupita kwina, ngati umo yakuchokela pa Ambuye, uyo ndi Roho.

Chapter 4

1Chapano, kwa chifukwa tuli ndi huduma ii, ndi ngati ambavo talandila kulekeleledwa, sitidula nkumbila. 2Badala yake, takana njila lonche la manyazi ndi izozababisika. Situishi kwa chanje, ndi sitilitumia vibaya mau la Mulungu. KWa kupeleka uzene tujilangiza tuwefe kwa gniza la kila munthu pachigololo pa Mulungu.3Nampho ngati mau lanthu labisika kwa anyiwajape ovulala. 4Pakati pa kusankhula kwao, Mulungu wa pajiko pano wapumbamba, njeru zao izosinkulupalila. Matokeo ake, siakoza kuliona dangalila la mau la chitukuko cha Kristo, ambaye chifanizi cha Mulungu.5Pakuti situjitangala tawefe, nampho Kristo Yesu ngati mbuye, ndi ife tawefe ngati atumiki wanu kwa njila ya Yesu. 6Pakuti Mulungu ndeuyo wadakamba, "dangalila siliwale kuchoka kumdima." Wawala mkati mwa mitima yatu, kuchocha dangalila la njeru ya chitukuko cha Mulungu mkati mwa kukalapo Yesu Kristo.7Nampjho tuli ndi kusungila uku mkati mwa vyamba va donthi, ili kuti ieleweke kuti mphavu yaikulu sana ndi ya Mulungu ndi osati yathu. 8Tuzunjika kupitila kila mtundu, nampho sitichochedwa, tiana mantha nampho sitijalidwa kudula kumbula. 9Tutesedwa nampho siadatutelekeze, tutaidwa panchi nampho sitiangamizidwa. 10Siku zonche tutenga mkati mwa nthupi latu nyifa ya Yesu, ili uti umyo wa Yesu uonekanencho mkati mwa nthupi lathu.11Ife tuli amayo siku zonche tachochedwa kufa kwa chifukwa cha Yesu, ili kuti umoyo wa Yesu uonekane kupitila matupi yathu ya kibinadamu. 12Kwa chifukwa ichi, nyifa ichita nchito mkati mwathu, ila umoyo uchita nchito mkati mwanu.13Nampho tuli ndi mizimu iija ya chikhulupi kulingana ndi chija chalembedwa. "Ndidakulupalila, ndi mchimwecho ndidakamba." Ndi fencha tukulupalila, ndi mchimwechencho tukamba. 14Tujiwa kuti yujha wamuhyusha Mbuye Yesu siwahyushe ife pamoji nafe. Tujiwa kuti siwatupeleke ife pamoji ndi anyaimwe pakati pakalapo iye. 15Kila chinthu ndi kwa chifukwa chanu ili kuti kwa kadili ya mwa, umo uenea kwa wanthu ambili kuyamikila kuzidi kuongezeka kwa chitukuka cha Mulungu.16Mchimwecho situdula kumbilo, ingakale kwa kubwalo tichakaa kwa mkati tuchitidwa anyuani siku hadi siku. 17Kwa nyengo ii yaifupi, mateso yaya yayepu yatuandaa ife kwa chifukwa cha muyaya olemela wa chitukuka upunda vipimo vonche. 18Pakuti sitipenya kwa chifukwa cha vinthu ambavo vionekana, ila kwa chifukwa cha vinthu ivo sivionekana. Vinthu ivotukoza kuviona ndi vantai pe, ila vinthu ova sivionekana ndi va muyaya.

Chapter 5

1Tijhiwa kuti ngati maskani ya jhiko yayo tilama umo yawanangidwa, tilinao jengo kuchoka kwa Mulungu. Ni nyumba iyosiidakonjedwe kwa manja ya binadamu, nampho ni nyumba ya muyaya, pakati pa ntambo. 2Pakuti pakati pa hema ili tidwala, tikakhumbila kurekedwa kwa maskani yathu kumwamba. 3Tikhubila kwa hifuko ichi kwa ndande yoivala sitionekana tili maliseche.4Kwa chazene nyengo tili mkati mwa hema ili tidwala tikalemeledwa. Sitifuna kuvuklidwa. Pothela pake, tifuna kuvekedwa, kuti chijha chafa chikhoze kumezedwa ndi umoyo. 5Yujha wadatikonja ife kwa chinthu ichi ni Mulungu, iye wadatipacha ife mzimu ngati chilango cha kale ichosichijhe.6Kwa chimwecho mukhale ndi kulimbikila siku zonche, mukale maso kuti nyango tili kukomo pakati pa thupi, tili kutali ndi Ambuye. 7Pakuti tienda kwa chikhulupi,opande koona. Kwa chimwecho tili ndi kulimbikila. 8Ni mbasa tikhale patali ndi kuchoka kutupi ndi kukhomo pamojhi ndi Ambuye.9Kwa chimwecho tiichita kuti chikhulupi chathu, ngati tikhala kukhomo kapena kuali, timkwadiiche iye. 10Pakuti lamulo taonche tionekane pachogolo pa mpando wa malamulo ya Kristo, kuti kila mmojhi wakhoze kulandila kila icho chifunika. Kwa vinthu ivo vichitika pakati pa thupi, ikakala ni kwa ubwino kapena kwa kuipa.11Kwa icho, kwa kuyajhiwa mantha ya Ambuye , taakhumbilicha wanthu. Umo tili, ionekana wazi ndi Mulungu. Niganizila kuti niveka. 12Sitiesa kukhumbilichani anyaimwencho ktiona ife ngati azene. Pambuyo pake tikupachani anyaimwe ndande ya kunyada kwa chifuko chathu, kuti mukhoze kukhala ndi yankho kwa wajha anyadila kukhuza kuonekana nampho opande chijha chili mkati mwa mtima.13Pakuti ikakhala ngati tadummphidwa ndi njelu, ni kwa chifuko cha Mulungu. Ndi ngati kuchokela kunjelu zathu zo kwana, ni kwa chifuko chathu. 14Pakuti chikondi cha Kristo chitilamula kwa chifuko tili ndi ili: Kuti munthu mmojhi wadafa kwa ndande ya onche, ndi kwa chimwecho onche afa. 15Ndi Kristo wadafa kwa ndande yaonche, kuti nywaja alama asadalamancho kwa chifuko chao achinawene. Pambuyo pake, lazima alame kwa ndande yake iye uyo wadafa ndi kuhyuka.16Kwa ndande ii, kuyambila saino ndi kuendekela sitimlamula munthu kulingana ndi khalidwe la binadamu, ingakale yapo hti tidampenya Kristo pakati pa namna ii. Nampho saino sitimlamula waliyonche kwa mate iincho. 17Kwa chimwecho ikakhala munthu waliyonche wali mkati mwa Kristo, iye ni chiumbe cha nyuwani. Vinthu vakale vathopita. Penya, yakhala ya nyuwani.18Vinthu vonche ivi vichoka kwa Mulungu. Wadativani chana ife kwa iye mwene kupitila Kristo, i watipacha mathandizo wa kuvanichana. 19Imeneyo ni kukamba, pakati pa Kristo, Mulungu walivanichana jhiko kwake mwene, opande kuwelenga kulakwa kwao pakati pao waikiza kwanthu nkhani ya kuvanichana.20Kwa chimwecho tisankhulidwa ngati awakilishi wa Kristo, kuti ngati Mulungu wamachita lufaa yake upitila ife. Tukupemphani anaimwe kwa chifuko cha Kristo: "Mvanichidwe kwa Mulungu!" 21Wadamchita Kristo kuti anchembe kwa ndande ya machimo yathu. Iye nuyo siwadachite machimo wadachita chimwechi kuti tikhoze kuchita haki ya Mulungu pakati pa iye.

Chapter 6

1Kwaicho kuchita nchito pamoji, tikupemphani msaandila madaliso ya Mulungu chabe. 2Pakuti wakamba, pa nthawi yavomeleka ndidali maso kwanu, ndi patsiku la kupumucha ndida kuthandizani. 3Sitiika mwala chekheleza munthu waliyonche, ndande sitifuna nchito yathu ikale yovekela kuipa.4Pambuyo pake, timajisonyeza tachinawefe pa vochita vathu vonche,kuti tili atumiki a Mulungu. Tili atumiki aiye mwaunyinji ndi molimbikila, masaucho, zowana ndi lamidwe lolimba. 5Kumenyedwa, kumangidwa chipwirikiti mkati mogwira nchito kwa mphamvu, osagone litulo usiku, ndi mkati mwa njala. 6Pakuyera, pakujiwa mozama, pakulimba mtima pakukoma mtima, mkati mwa mzimu oyera ndi mwachikondi chosanyenga. 7Tili atumike wake mkati mwa mau lazene mkati mwa mphamvu za Mulungu. Tili ndi zia za chilungamo chifukwa cha janja la kwene la manjele.8Tichita nchito molemekezedwa ndi monyozedwa ndi monyozedwa, mkati mokambidwa kuipa ndi kuelekeledwa. Tikambidwa kuti aunami nyengo ife azene. 9Tichita nchito ngati sitijiwika nditikali osajiwike bwino, tichita nchito ngati yao amwalila ndiona tikali ndi moyo. Tichita nchito ngati anyiyao alangidwa ndande ya vichito vathu nampho osati ngati yawo alamulidwa mbaka na kumwalila. 10Tichita nchito ngati wanthu amadandaulo, nampho nthawi zonche tili achimwemwe. Tichita nchito ngati wanthu opande kanthu, nampho tilemelecha ambili. Tichita nchito ngati kuti sitipeza knthu ingakale tili ndi vinthu vonche.11Takukambilani uzene wonche, Akorintho ndimitima yathu ya masuka. 12Mitima yanu sichekelezedwa ndi ife, ikapanda mchekelezedwa ndi maganizo yanu mwachinawene. 13Chipano pakusinthana mwa chilungamo ndi kamba ngati kwa wana masulani mitima yanu bwino.14Musagwirizana pamoji ndi yawo sakulupirila, pakuti pali chigwiliano chanji chilungamo ndi machimo? Ndikuti chigwilizano chanji kwala ndi mdima? 15Ndi mavanichano yanji Kristo wakhoza kukhala nayo ndi beriali? Kapina uyo wakuluparila wali ndi malo yanji ndi osakulupalle? 16Ndi kulimanavanichano yanji pakati pa nyumba ya Mulungu ndi chifani? Pakuti ife nde nyumba ya Mulungu wali wa moyo, ngati umo Mulungu wadakambila. Sindikale nawo ndi kumaenda nawo. Sindikale nawo sakhale wanthu wanga.17Kwaicho, chokani mkati mwao, ndimkakhale patali nawo, akamba Ambuye. Msagwira chinthu chosayera, ndisindikula ndileni. 18Sindikale tate wanu, namwe simkhale wana wanga wachimuna ndi wachikani akamba Ambuye.

Chapter 7

1Okondedwa wanga, pakuti tili n chilanga ichi ndi kujichuka tachinawefe kwakila chinthu ambacho litichita kukala akazuzu kupitila matupi yathu ndi kupitila mzimu, ndi tuufunefune mzimu oyela kupitila mantha ya Mulungu.2Chitan nafasi kwa chifuko chathu! Sitidamlakwile munthu walienche sitidampweteke munthu walienche. 3Nikamba ili osati kwakukulaumuni pakuti natokamba kuti mmene mmitima mwathu, kwathu ife kufa pamoji ndi kulama pamoji. 4Nili ndi ujasili wambili mkati mwanu, ndi nili ni malinga kwa chifuko chanu najala ndi chisangalalo, ninkala ndi chimwemwe ata pakati kati pa mazunjo yathu yonche.5Todaja Makedonia, mathupi yathu siyadali ndi kupumulila, pambuyo pake tidapeza mazunjo kwa nman zonje kobulidwa nkondo upande wakubwalo ndi mantha upande wa mkati. 6Nampho Mulungu, uyowathondoza nyao adula tamaa, wadanthondoza kwa kuja kwa Tito. 7Siidakale kwa kuja kwake tu kuti Mulungu wadatitondoza. Idali ni chisangalalo cha Tito izo wadalandila kuchokela kwanu. Iye wadatikamila chikondi chachikulu icho mulinacho, madandaalo yanu, ndi umomdali ndi mantha mantha kwa chifuko changa chimwecho naidi kukala ndi chisangalalo kupunda.8Ata ingakale waraka wanga udakuchitani kudandaula, ine siniudangdaulila, nampho niudandaulila nyengo yaponidaona waraka umene uo udawachita anyaimwe kukala ndi madandaulo. Nampho nadali ndi madandaulo kwa nthawi ya ifupi. 9Chipano nili ni chisangalalo, osati kwa chifuko mdali ndi vuto, nampho kwachifuko madandaulo yanu idakuplekelekelani kuli toba, mdapatikana ndi madandaulo ya kiungu, chimwecho mdateseka osati kwa hasara kwa chifuko chathu. 10Pakuti madandaulo yakiungu ipeleka toba ambayo ikamilisha uwokovu bila a kukala ndi mavuto, adandaulo ya pajiko, hata chimwecho, ipeleka umauti.11Penyani madandaulo yaya yakiungu udabalicha azma yanji yaikulu mkati mwanu, jinsi yanji azma idali yaikulu mkati mwanu, mantha yanu, makumbilo yanu, bidii yanu, ndi hamu yanu kuona kuti haki ifunika kuchitika! Katika kila chinthu mwasibitisha machinawene kukala ndi. 12Ingakale nidakulembelani anyaimwe, sinidalembe kwa chifuko cha olakwa, wala osati kwa munthu uyowatesedwa ndi n voipa. Nalemba ili kuti uzene wa mitima yanu kwachifuko chathu ichitidwe kujiwika kwanu pachogolo pamaso ya Mulungu.13Ni kwa chifuko yoichi kuti titondozedwa, kupitila nyongeza yachimwemwe chathu tachinawefe, tisangarara ni hata zaidi kwa chifuko cha chisngaralo cha cha Tito, pakuti mzimu wake idasangalala ndi anyaimwe onche. 14Pakuti ngati nidali ni malinga kwake kuhusiana ndi anyaimwe, sinidali ndi nchoni kinyume chake,ngati kila mau ilotidalikamba kwanu lidali lazene, maringa yathu kuhusu anyaimwe kwa Tito yadasibitishidwa kuti ya zene.15Chikondi kwake kwa chifuko chanu ata ni wamkulu kupunda, ngati ukumbukila utii wanu mwaonche jnsi umodamkalibisha iye kwa mantha ndi kutenthemela. 16Nili ndi chisangaralo kwa chifuko nili ndi ujasili okamiika mkati mwanu.

Chapter 8

1Tikufunani anyiimwe mjiwe, kaka ni dada, kuhusu mwawi wa Mulungu ambo wachochedwa kwamakanisa ya Makedonia. 2Muda wa yeso la likulu la mazunjo, kuchuluka kwa chisangalalo chao ni kuongezeka umphawi wao, kwa bala chuma chachikulu cha kukaribisha.3Chifuko nishuhudia kuti adachocha kadiri ya umoadakozela, ni ata zaidi ya umoadakozela. 4Ni kwa kufuna kwao achinawene ka kutupempha kwa mbili, atupempha kwa chifuko kwa ntando ya umoja katika utumiki uu kwa okulupalila. 5Ii siidachokele ngati umo amaganizila. Badala yake, poyamba adajichocha anyiio achinawene kwa Ambuye. Pambuyo adajichocha anyiio achinawene kwatu kwa kumkonda Mulungu.6Chimwecho tidamphempha Tito, wadali tayari, wa, wayembicha nchito ii, kupeleka katika kukamilika jambo ili la kukarimu juu yanu. 7Nampho anyiimwe muli ni vambili katika kila chinthu, katika chikhulupi, katika kukama, katika kujiwa, katika kujituma, ni katika chikondi chanu kwa chifuko chatu. Chimwecho mpenyelele kuti anyiimwe mkala ni vambili katika jambo ili la kukaribisha.8Nikamba ili asati ngati lamulo. Badala yake, nikamba ili dala kupima uzene wa chikondi chanu kwa kulinganisha ni hamu ya wanthu wina. 9Kwa chifuko mjiwa mwawi wa Ambuye watu Mpulumusi, ata ngati adali ni chuma, kwa chifuko chanu adali amphawi. Dala kuti kupitila umphawi wao mkoze kukala ni chuma.11Katika jambno ili nikupacheni ganizo ambalo likuta ngatileni. Chaka chimoji icho chapita, simdayambe twe kuchita chinthu. Nampho mdakumbila kuchita. 10Chapano likamilisheni ngati tu uotidali ni hamu ni kulifuna kuchita, nampo bwanji, mdakakoze pia kulipeleka katika kukamilika kwa jinsi umo mkozela. 12Pakuti muli ni hamu yochita chinthu ichi, nin jambo la bwino ni livomeleka. Lazima liime juu ya chija walinacho munthu, osati juu ya chija walije munthu.13Pakuti nchito ii osati chifukwa chakuti wina akoze kupaunafuu manyiimwe mkoze kulemekeledwa baadala yake kukale ni usawa. 14Ukulu wame wa muda wa saino utangatile kwa chija achifuna. Ii ni chimwecho pa dala kuti ukulu wao ukoze kutangatila vofuna vanu, ni kuti kukale usawa. 15Ii ni ngati umoyalembedwela, "iye wali ni vambili siwadali ni chinthu chalichonche chakala ni iye wadali ni chaching'ono siwadali nikufuna chalichonche."16Nampho wayamikidwe Mulungu, waika mkati mwa mtima wa Tito mtima uja wa kujituma wa kujali ambayo nilinayo chifukwa chanu. 17Pakuti osati tuu wadalandika mapemphelo yatu bali pia wadali ni kujituma kujituma kulingna ni mpemphelo yameneyo. Wadaja kwanu kwa kufuna kwake mwene.18Tamtuma pamoji naye m'bale ambaye amsitia pamoji ni makanisa kwa chifuko cha nchito yake katika kutangaza mau. 19Osati chimwechi tu, nampho pia wadasankhidwa ni makanisa kupita ni ife katika kulitenga malo yosiana siana tendo ili kukaribisha ili ni kwa ufulu wa Ambuye wene ni kwa hamu yatu ya kutangatila.20Tikwepa kukozekana kuti waliyonche nikoze kulalamika kuhusu ife ni kuhusu kukarimu uku ambako tikutenga. 21Titenga kupenyelela kuchita chiticha ulemu , osati tu pamaso pa Ambuye, nampho pia pamaso pa wanthu.22Pia timtuma m'bale mwina pamoji nao. Tampima mara za mbili ni tamuone ni uyo wali ni hamu kwa chifuko cha nchito za ambili. Ata saido wali ni kujituma kwa mbili kwa ndande ya kuji kulupalila kwa kukulu kwa kukulu walnako mkati mwanu. 23Kwa nkhani ya Tito, ye ni otumika ni njanga ni ochita nchito mnjanga kwa chifuko chanu. Ngati kwa abale watu, atumidwa ni makanisa ni aulemu kwa Mpulumusi. 24Chimwecho alangizeni chikondi chanu, ni mulangize kwa makanisa ndande ya kujiona kwatu kwa chifuko chanu.

Chapter 9

1kufunikilana ndi chifandizo kwa chifuko cha okurupilila palibwino kupunda kwaine kukukambilani. 2Ndijiwa kupitila chofuna chanu, chimondi kulupalicha wantu akumake dunia, ndida akambila kutu akaya idali tayali kuyambila chakachota kufuna kwanu kwa kupachani mtima ambili anu kuchita.3Chapano naatumiza achaabale wanga dale kuti kujichita kwanu kupitila anyiimwe sikudakala kwa chabe ndi dale kuti kuti mkadakala tayari ngati mmo ndidakukambila mkadali. 4Mwena mwake ngati muntu waliyenche wa ku Makedonia siwafike pamoji ndi anyaimwe ndi kukupezani simdaji kazikiche, tikada yaona yaya sindikamba chilichonche kupitila anyaimwe pokala olimba mtima pakati pa anyaimwe. 5Mmwemo ndidaona idali chamate kukupepesani achabale kuja kwanu ndikuchita makonjedwe mwamsanga chifuko cha mpaso.6Imene mdalenjeza lindimmwemo dala kuti zikale zakonjeka ngati mwawi nafencho ngati chinthu chalamulidwa. Ganizo lilili muntu wa vyala vochepa siwakolole vochepa nayoncho wavyala kwa mtundu wa mwawi siwakolole kwa mwawi. 7Mmwemo waliyenche wachoche ngati umo wakonjela mumtima mwake mmwemo nayenche siwadachoche kwa madandaulo kapena kwa kukakanizidwa pakuti Mulungu wamkonde uja wachocha kokondwela.8Ndi Mulungu wakoza kukonjelea mwawi kwa chifuko chanu dala kuti ntawi iliyenche pakati pankani zonche mkoze kupeza vo funa vanu ichi sichikale dala kuti mukoze kuonezela mtundu wochita vabwino. 9Ningati mmene yalembedwela "wamwala kwina kwake ndikuuchocha kwa wantu otedwa, ubwino wake okala wosata."10Nayenche wachocha mbeu kwa ovyala ndi mkate chifuko chakudya mmwemo siwachoche ndikuonjezela mbeu yanu chifuko cha kuvyala iye siwaonjezele uo kolola vya ubwino. 11Simpezi kuwina kwa mtundu walionche dala kuti mkale wantu wa mtima wa bwino ichisidipeleke mpaso kupitila ife.12Pochita chitandizo ichi osati kuti itandiza vofuna vya okurupalile ionjezela pakati pa vichito vambil va mayamiko kwa Mulungu. 13Chifukocha kuezedwa kwanu ndi kuvomelezedwa patandizo ili simkweze Mulungu kwa kujichicha kwa kuvemela kwanu kwa injiri ya Kristo mmwemoncho simkwezeke mulungu kwa chilengedwe chanu kaanyaiwo ndi kwa waliyenche. 14Akukumbilanu ndiupemphani chifuko chanu nchita chimwechi chifuko cha mtendele wa ukuru uli pamwamba panu. 15Mayamiko yakale kwa Mulungu kwa chfuno chake chosakambilika.

Chapter 10

2Ine Paulo namwene nikuchisani mojichicha mwa Kristo, ine ndi ochika nyengo nikala kwanu, nampho nikala olimbikila kwanu nyengo nikale kutali na anyiimwe. 1Nikupemphani kuti nyengo nikala pamoji na anyiimwe sinifuna kukala olimbikila ndi kujikulupilila namwene nampho niganiza nifunika kukala olimbikila yapo nikangana ndi anyiawo aganiza tikala kwa mtundu wa tupi.3Pakuti ingakale tujenda mwa tupi, sitibulana nkhondo mwa mtundu wa tupi. 4Pakuti zidatibulila osati za tupi, pambuyo pake zili ndi mphavu zowananga chilindo kuchocha machezel yosowecha.5Nditu, tiwananga ndi kugwecha maganizo ndi chilichonche chikuzika mwa malango ya Mulungu, titena mphavu zonche ndi maganizo ya mdani kuti zilemekeze Kristo. 6Ulemu wanu ukakwanila, sitiwanange kila chichito chilibe ulemu.7Yapenyeni yaya yali pachogolo pa maso yanu, walionche wakajiona iye ndi Wakristo, waganizila kuti ife nafe tili ngati iye Wakristo. 8Ingakale napunda kujidama pang'ono, kukuza malamulo yamene Ambuye atipacha tikilimbikicheni osati kukugomolani, siniona nchoni.9Sinifuna ichi chioneke kuti nikuofyani ndi kalata zanga. 10Munthu wakoza kukamba "kalata za Paulo ni zolemela, nampho mwene yapo wakala pamoji ndi ife ndi munthu opande mphavu, ndi mau yake yalibe kanthu."11Wanthu amtundu umene, afunia kujiwa kuti icho tilemba mkalata tili kwa kutali chili ngati chimene tinena tikakala pamenepo. 12Sitipita kwa kutali, ngati kujikusa achinawene kapena kujifananicha achinawene na anyiwaja ajielekela mmoji alibe njelu.13Nampho ife sitikoza kujielekela mopitilila, kujielekela si kukale mwa chimene watipacha ulungu , mbaka kufika kwanu. 14Sitidalumphe malile tidaikidwila nyengo taja kwanu, ife tidali oyamba kuja kwanu tiakupelekelani utenga wa bwino wa Kristo.15Kwa icho sitikoza kuchitila dama nchito achita wina, koma tikulupilila kuti chikulupi chanu sichipunde mkati mwanu kuchatana ndi umoatiikila Mulungu. 16Pamene sitikoze kuulalika utenga wa bwino mmaiko ina kutali na anyiimwe, ndi siikala nchito yojidamila iyo achita wina kumalo kwina17Nampho ngati umo yakambila malembo, "uyo wajidama ndi wajidamle nchito ya Ambuye." 18Uyo wavomelekosati yuja wajielekela mwene, koma uyo waelekeledwa na Ambuye.

Chapter 11

1Ndisi kuti mdavavumilia ndi ine pakati pa ochepa pa upumbavu. Nambo pauzene mulimbikila ndiine. 2Pakuti muli ndiwanjaje kupitila imwe ndili ndijanje ya Mulungu pandande yanu, choka wapo wadakulengezani imwe paukwati wawamuna moji, ndida kuaidini kukupelekelani anyiimwe kwa Kristo ngati bikira wa bwino.3Nambo ndiopa kuti pandande fulani, ngandi njoka umo idamnyengela Eva pa hila yake, makhanizo yanu yakoza kunyengedwa kutali kuchoka kumapemphelo yauzene kwa Kristo. 4Pakuti kwa mfano kuti mundu fulani wadaja ndi watangaza Yesu mwina opande yuja tidakulalikilani pena kwa mfano kuti mkalandila mtima winajo kusiyana ndi yuja wadalandila injili inajo yosina ndi ifa mudailandila. Mudalibikila vindu ivi vabwino vikwana!5Pakuti nikhaniza kti ine opande mmitima mwaali pajiko payao aitanidwa otumidwa abwino. 6Namba atangati ine sinidayualuzidwe kuchoka pembelo, oande chochi pakati pazelu. Kwakila njila ndi pakati pavindu voje talichita ili kujiwikana kwanu.7Bwa, nditachita chimo pa kujipepelecha namwene ili anyiimwe mukoze kwezedwa? Pakuti ndimalalika kosiidwa injili ya Mulungu wanu. 8Ndidalanda makanisa yambili kolandila msaada kuchoka kwao ili nkuti ndidakakoza kukuudumiani anyiimwe. 9Pandawi nili namwe ndinidali pakati pofuna, sindidamsiile walionje. Pakuti zofuna zanga yadakwanichidwa ndaabale yoadaja kuchoka Makedonia pakati pa kila chindu najibisa namwene kutokukala mzigo kwanu, sindiendekele kuchita chimwecho.10Ngati uzene wa Kristo yuli mkati mwanga, uku kujikweza kwanga,sikukalichidwa chete pakati pamalo pa Akaya. 11Ndande yanji? Pandande sinikukondani? Mulungu wajiwa ndikukondani.12Nambo chija ndichichita, sindichichiteja sindichichi kuti ndikoze kuziba malo yawaja akumbila malo yakuji ngati umo tili pakati chichija ichokulupilila. 13Pakuti wandu waja ndiotimidwa atila ndi opotanjito zonyenga, ajinganamula wene ngati otumidwa Akristo.14Ndi iyi sidabwicha, pakuti ata satana wajing'anamula mwene ngati angelo owela. 15Iyi ilibe kudabwicha chalikulu ngati otumidwa wake nao ajinganamula wene ngati otumidwa auzene mmatelo mwao sikale ngati machitidwe yao umoyafunika.16Ndikambajo: basi wasadakalapo ndi mundu walionje uyowakhaniza ine apusa. Nambo ngati simuchite, ndilandileni ine ngati opusa ili ndikoze vujikuza pang'ono. 17Chija ndikamba kuhusu uku kujikulupilila ndi kujiona sikueluzidwa ndi Ambuye, nambo ndikamba ngati opusa. 18Pakuti wandu ambili ajiona panjila ya tupi, sindi onenjo.19Pakuti mudatengelana patendele ndi opus, anyiimwe nawene olemekezeka! 20Pakuti mudatengelana ndimundu ngati wakakutila kotumidwa, ngati isababisha kugawanyika pakati panu, ngati sakutumieni anyiimwe pafaida yake ngati sajiike pamwamba pahewa, pena ngati sakumenyeni pamaso. 21Sindikambe panjoni yatu kuti sitali olepela kupunda kuchita chocho nditikali ngati walionje siwajone ndikamba ngati chilekwa inenjo sinione.22Bwa, anyiiwo ndi Ayahudi? Ndi ine ndicho. Bwa, anyiiwo ndi Aizraeli? Ndi ine ndi chocho. Bwa, anyiiwo ndi chibadwa cha Iburahimu, ndiine ndi chocho. 23Bwa, anyiiwo ndi otumidwa a Kristo? (ndikamba ngati nidalumbidwa ndi zelu zanga) ine ndikupunda. Nakula ata pakati pa njito zolimba kupunda, kutali kupunda kukala komangidwa pakati pobulidwa kuta vipimo, pakati pojilimbicha kunyifa.24Kuchoka kwa Yahudi namlandila mala kamoji ndidalidwa myaka. 25Mala kaktu ndidapuku mmeli ndatumila usiku ndi usana mnyanja wazi. Ndakala paulendo wandawi zose, paulendo wa muchinje, paulendo wambava. Paulendo ochoka pawandu wanga wene, paulendo kuchoka kwa wandu amjiko, paulendo wamji, paulendo wajangwa, pakati paulendo wanyanja, kuchoka kwa abale atila. 26Ndakala pakati panjito zolemba, pakati pausiku wambili osagone, pakati panjala ndi lujo, mala zambili pakati pomanga, pakati pambepo ndi maliseche.27Ndakala pakati panjnito zolimba, pakati pansiku wambili osagone, pakati panjala ndi lujo, mala zambili pakati pomanga, pakati pambepo ndi maliseche. 28Patali pavila chindu china, kuli misukosuko wakila nyengo yangu yo kulikilidwa kwanga pandande ya makanisa. 29Ndiyani opepela, ndiine opande opepela? Yani wachiticha mwina kungwa muzambi ndiine sindidwala mnyumba?30Ngati ndizoona ndijione sindivumie kuita chija ichochiangiza kupepea kwanga. 31Mulungu ndi atate wa Mbuye Yesu, iye uyowalemekezedwa muyaya, wajiwa kuti ine sininyenga.32Kuja Kudameski,wakulu wa mkuwa panji pa mfalume aletawaali ndiwa usunga muji wa Dameski ili kunigwila. 33Nambo ndidaikidwa museche, kupitila padilisha pakati papupa, ndi ndidapukwa kuchoka mmanja mwake.

Chapter 12

1Ndi lazima ndijivune, nampho palibe ichochiongezedwa ndi limenelo siniendelee kurosa ndi kumasura kuchoka kwa Ambuye. 2Ndimjiwa munthu mmojhi pakati pa Kristo ambaye vyaka kumi ndi vinai iyoyapita ambayo ikakala. Mkati mwa nthupi, au kubwalo kwa nthupi, ine sindijiwa, Mulungu wajiwa - uyowanyakutidwa pamwamba, mkati mwa kumwamba kwa katatu.3Ndi nijiwa kuti munthu uyu - ikakala mkati mwa nthupi, au kubwalo kwa nthupi, ine sinijiwa, Mulungu wajiwa. 4Ndi wadatengedwa pamwamba hadi paradiso ndi kuvela vinthu voele sana kwa munthu waliyonche kuyakamba. 5Kwa niaba ya munthu ngati uyu sindijivune, nampho kwa niaba yanga namwene si ndijivuna, ingakale kuhusu udhaifu wanga.6Ngati nifuna kujivuna, sindi dakakala mpumbavu, pakuti ndimakakamba uzene. Nmpho sindisiye kujivuna ili kuti wasidakalapo waliyonche uyosiniganizilike zaidi ya yameneyo kuliko ichochionekana mkati mwanga au kuvela kchoka kwanga. 7Sindijivunancha kwachifukwa cha yameneyo yomasulidwa ya aina ya kudabwicha. Chipano, mchimwecho sindijalidwa ndi kiburi, minga idaikidwa mkati mwa nthupi langa, mjumbe wa satana kunivamia ine, ili sinidang'anamuka kukala wa majivuno.8Mara katatu ndidamphempha mbuye kuhusu ili, ili iye wauchoche kuchoka kwanga. 9Naye wadanikambila, "Neema yanga itosha kwa chifukwa chaka, pakuti mphavu ichita bwina pakati pa udhaifu. Mchimwcho, ndidakakhumbila zaidi kujivuna zaidi kuhusu udhaifu wanga, ili kuti kukoz kwa Kristo ukaze kukala pamwamba panga." 10Chipano nditosheka kwa chifukwa cha Kristo, pakati pa udhaifu, pakati patukanidwa, pakati pa shida, pakati pa mateso, pakati pa hali ya kuganizila pakuti nyengo ndili dhaifu, ndi pambuyo pake ndili ndi mphavu.11Ine ndili mpumbavu! Anyiimwe mdanilazimisha kwa limenelo, pakuti nidakasifidwa ndi anyiimwe, pakuti sindidali osuka kabisa kwa anyiyawo atanidwa atumiki - bwino, atangati ine osati chinthu. 12Kulangiza kwa uzne kwa atumiki kudachitika pakatikati panu kwa kuvumiliya, kulangiza ndi kudabwicha ndi vichito vavikulu. 13Kwa namna yanji mdali a muhim apanchi kuliko nyumba za mapemphlo izozakatila ingkale kuti sindidakale katundukwanu? Mundilekelele kwakosa ili!14Penya! Ine ndil tayari kuja kwanu kwa mara ya katatu. Sindikala katundu kwanu, pakuti sindifuna chinthu chili chanu, ndikufunani anyaimwe. Pakuti wana siafunikana kuika kana kuika akiba kwa chifukwa cha kwawakwa bala. Badala yake akwabala afunikana kuika akiba kwa chifukwa cha wana. 15Sindikale ndi mtendele zaidi kutumi ndi kutumikidwa kwa chifukwa cha mitima yanu, ngati ndi kukandani zaidi, ndifunikana kukondedwa pang'ona?16Nampho ngati umoili, sindida kulemeleleni katundu anyiimwe. Nampho pakuti ine ndi mwelewa sana, ine ndi yuja uyondidakugwilani anyaimwe kuti ndakala kuti ndakuninkhani kwa mtila. 17Bwa, nditatenga kwa kujichitila faida kwa waliyonche ayondidamtuma kwanu. 18Ndidamphempha lita kuja kwanu, ndi nidamtuma mbale mina pamoji naye. Bwa, Tito wadakuchitilani faida kwanu? Bwa, sitidaende mkati mwa mapazi yayaja?19Mganizila kuti nyengo ii onche tujitetea ife tawefe kwanu? Pachogolo pa Mulungu, ndi pakati pa Kristo, tukamba kila chinthu kwa chifukwa cha kukukwimichani anyaimwe.20PAkuti ndiopa kuti yaposindije ndikoza kukukosani anyaimwe ngati umaninkhumbila ndiopa kuti mkoza kunikosa ine ngati umo umomukumbila ndiopa kut kukoza kukala ndi mijadala, chanje, milipuko ya asila, nkumbia la kjiona, umbeya, kiburi ndi ndeo. 21Ndiopa kutindikoza kuganizilichidwa ndi ambili ambao achita chimo kabla ya chipano, ndi ambao sialapa uchafu, nchi chiwelewele ndi vinthu vankhumbila ila alichita.

Chapter 13

1Ii ndi ntawi ya katatu kuti ndikuja kwanu mlanduulionchelazima ukonjedwe ndi chilimbikicho cha amboni awili kapena atatu. 2Ndato kamba kwa acha ameneo achita machimo pambuyo ndi kwawena ntawi ndili kumeneko ntai ya kawili, ndi nikambacho yapo sindifikecho sindivumiliacho.3Ndikukabilani ili anyiimwe chifuko mfunafuna umboni kuti Kristo wakamba kupitila ine, iye osati walibe mpavu kwa anyiimwe pambuyo pake iye wali ndi mpavu mkati mwanu. 4Pakuti wadavuchitidwa pa mavuto yanu nampho wakali ndi pamvu za Mulungu pakuti ifenancho tilije mpavu mkatimwake nampo sitikale naye kwa mpavu za Mulungu mkati mwanu.5Jipenyeni mwachinawene mjipenye ngati muli ndi chikulupi jipenyeni mwa achinawene simjiwa kuti Yesu Kristo wali mkati mwanu? Iye walipo kapena ngati si mdachimikizidwe. 6Ndi ndili ndi mpavu kuti anyiimwe simjiwe kuti ife sitidakanidwe.7Chapano jipempa kwa Mulungu kuti simdakoze kuchita chilichonche choipa sindipempa kuti ife tikoze kupenyedwa taya pitila mayeso pambuyo pake ndipempa kuti mkoze kuchita chili chabwino ingakale kutijikoze kupenyedwa kuti talepela mayeso. 8Pakuti ife sitikoze kuchita chilichonche pambuyo pauzene nampo chifuko cha uzene.9Pakuti sangalala apo tikala tulije mpavu na mwencho mkakala ndi mpavu tipempa kuti mkozechedwa chichifidwe. 10Ndizilemba mkawizi pamene ndili patali ndi anyaimwe sindifuna kukulangizani kukalipa anyaimwe sindifuna kutumikila lamulo limene Mulungu wandipa cha ine ndikukonjeni osati kukuwanangani panchi.11Pambuyo pake apaie wa achimono ndiwa achikazi sangalalani chitani nchito chifuko cha kubwezedwela mtilidwe mtima mvemelezane mwaachinawene kwa mwachinawene mkale pamtendle ndi Mulungu wa chikondi ndi mtendele siwakale pamoji namwe. 12Mlonjelani kwa waliyenche kupenyana mmachakaya.13Chikhulupi onche akulonjelani. 14Mtendele wa Ambuye Kristo chikondi cha Mulungu ndi umoji wa Kristo ndi mzimu woyela ukale pamoji namwe mwaonche.

Galatians

Chapter 1

1Ine Paulo mtumiki. Ine osati mtumiki chekela kwa wantu kapena kupitila kwa wantu nampo kupitila kwa Yesu Kristo ndi Mulungu tate watu wadatizukiche kuchokela kwa wantu ade mwalile. 2Pamoji ndi abale wonche ndiine, ndi yalembelo mecha lichi ya Galatia.3Mtendele ukale kanu uchokela kwa Mulungu tata watu ndi Yesu Kristo. 4Wajichocha mwene wake chifuko cha machimo yanu dalakuti tiramichidwe ndi ntawi izi za mapichidwe kuchokela ndi chikondi cha Mulungu watu ndi atate. 5Kwaiye uale ndi ufuru ntawi nsonse.6Ndizizwa kuti mng'ana mukilila na mwamsanga ku uhaliki wena ndizizwa kuti mng'ana mukililana patali kuchokela kwaiye mwene wakutanani kwa mosaganizila mwa Kristo. 7Kulibe uhalikiwena nampo kw wantu wochepa akuchitichani anyiimwe mavuto ndi kufuna kuugana mula ulaliki wa Kristo.8Nampho atangati ife kapena angelo kuchokela kumwamba sialalikile kwanu ulakaliki osimpana ndi uja tia lalikila kwan walengedwe. 9Ngati umo tidakambila mmayambo, ndi chapano ndi kamancho ngati pali muntu siwalalikilencho ulalki yo simpana ndiumo mwailandilila walengedwe. 10Kwani chapanolino ndifunafuna chizindikililo chawante kapena Mulungu ndifuna kwa osangalalicha wantu? Ngati ndi yendekela kuyesa kwa asangalalicho wantu ine osati mtumiki wa Kristo.11Abale ndifuna kuti anyaimwe muhiko kuti ulalki ndalalikila siuchokela ndi wanthu. 12Sindidalandile kuchokela kwa munthu kapenasindida yakuzidwe. Pambuyo pake idali kwa ulangize wa Yesu Kristo kwaine.13Mdatovela pakati pamalamidwe yanga yambuyo pakati pa dini ya Kiyahudi mmenemo ndidali adinivuticha wntu kwa kukalipila kanisa la Mulungu kupunda chipimo kwano ngilatu. 14Ndidali ndi ndiendekela pakati padini Yakiyahudi kupunda acha abale ambili Wayahudi ndidali olimbikila kupunda pakati pa masombo wa anya atate wanga.15Nampo Mulungu wadekoade kunisaukula ine kuchokela mmimba mwa amaye. Wadanditana ine kupitila mwawi wake. 16Kumkwimicha mwana wake mkati mwake dalakuti ni mlengeze mkati mwa wantu wake ajiko kapena singida funefune ganizo la tupi ndimwazi. 17Ndi sindida kwele kupita Kuyerusalemu kwa anyiwaja adali atumika pambuyo paine pambuyo pake ndidapita Kuuarabu ndi pambuyo kubwela Damesiki.18Pambuyo pauyaka vitatu ndide kwela kupita Kuyerusalemu kumuyendela Kefa ndidekale naye masikio kuani ndeya sano. 19Nampo sindidaone otumidwa wena ikapanda Yakobo mbale wake ndi Mulungu. 20Penyani pachogolo Pamulungu sindinamiza kwa chimene ndi chilemba kwa anyaimwe.21Pambuyo pake ndidapita kumikoa ya Shamu hadi Kilikia. 22Sindimajiwike kwa maso ndi akanisa ya kwa Ayahudi yaja yadali pakati pa Kristo. 23Nampo adali ndiaveri tu, "iye wadali ndiwativuticha chapano walengeza chikurupi wamachi wananga." 24Adali ndi amkwezeka Mulungu chifuko chaine.

Chapter 2

1Baada ya vyaka kumi na nne nidapitancho Kuyerusalemu pamoj ni Barnaba. Pia nidamtenga Tito pamoji ni ine. 2Nidapita kwa ndande Mlungu wadajilangiza kwanga kuti nidafunka kupita. Nidaika pachogolo pao mau ambalo nidalitangaza kwa wanthu osamjiwa Mlungu. (Nampho nidakamba kwa chisisi kwa anyiyao idajulikana kuti ochogoza atumika). Nidachita chimwechi dala kuhakikisha kuti sinitamanga, au nidatamanga chaje.3Nampo ata Tito, wadali pamoji ni ine, wadali Myunani, wadalazimishidwa kuswedwa utonga. 4Jambo ili lidachokela kwa ndande ya abale aunami adaja kwa chisisi kupeleleza uhuru tilinao katika Mpulumusi. Adakumbila kutuita ife kukala mbowa wa lamulo. 5Tidajichoche kwalemekeza ata kwa saa imoji, dala kuti mau la zene likale bila kung'anamuka kwanu.6Nampho anyiwaja akambidwa kuti adali ochogoze adatangatile chalichonche kwanga. Chalichonche adali amachichita sichidali ni mate kwanga Mlungu siwavomela kpendelea kwa wanthu. 7Badala yake adaniona kuti nakulupalilidwa kulitangaza mau kwa anyiyao ambao adaswedwe utonga. 8Kwa chifuko Mlungu, wadachita nchito mkati mwa Petro kwa chifuko cha ulaliki kwa anyiwaja aswedwa utonga, pia wadachita nchito mkati mwanga kwa wanthu osamjiwe Mlungu.9Muda Yakobo, Kefa n9i Yohana, adajulikana kuti alimanga kanisa, adajiwa mwawi napachidwa ine, adatulandila katika umoja ineni Barnaba. Adachita chimwechi dala kuti apite kwa wanthu osamjiwe Mlungu, midala kuti akoze kupita kwa anyiwaja aswedwe utonga. 10Pia adatufuna ife kwa kumbukila amphawi. Ine pia nidali nikumbila kuchita jambo ili.11Muda Kefa wadaja Antiokia, nidampinga waziwaz kwa ndande wadali walakwila. 12Kabla ya wanthu fulani kuja kuchoka kwa Yakobo, Kefa wadali wakuja pamoji ni wanthu osamjiwe Mlungu. Nampho anyiyawa wanthu yapo adaja wadasa ni kuchoka kupita ni kuchoka kwa wanthu osamjiwe Mlungu. Wadali waopa wanthu ambao adafuna kuswedwa utonga.13Nchimwecho Wayahudi wina adavomelezana ni unafiki uu pamoji ni Kefa. Matoeo yake yadali kuti ata Barnaba wadaengedwa ni unafiki wao. 14Nampho yapo nidaona kuti adali siachata mau ya zene, nidamkila Kefa pamaso pao onche, "ngati anyiimwe ni Wayahudi nampho mkala ni vichito va wanthu osamjiwe Mlungu badala ya vichito va Kiyahudi, ndande chiani mwalazimicha wanthu osamjiwa Mlunu kukala ngati Wayahudi?"15Ifetili Wayahudi kobadwa ni osati, "wanthu osamjiwe Mlungu ali ni chimo." 16Jiwani kuti palije wawelengedwa mzene kwa vichito va lamulo. Badala yake, awelengedwa uzene kwa chikulupi mkati mwa Mpulumusi dala kutitiwelengedwele uzene kwa chikulupi mkati mwa Mpulumusi ni osati kwa vichito va lamulo. Kwa vichito va lamulo palije tupi ilo liwelengedwele uzene.17Nampho ngati yapo timfunafuna Mlungu kotuwelengela uzene mkati mwa Mpulumusi, tijipeza techinawene pia kuti tili i chimo. Bwanji mpulumusi wadaitidwa mbowa wa chimo? Osati chimwecho! 18Chifuko ngati nimange kulupalilo langa juu yopenyelela lamulo, kulupalilo ambalo nidatolichocha, nijilangiza namwene kuti olakwida lamulo. 19Kupitila lamulo nidaja kwa lamulo, kwa icho ifunika kukala kwa cha Mlungu.20Nawambidwa pamoji ni Mpulumusi. Osati ine niala, ikapanda mpulumusi wakala mkati mwanga. Maisha nikala katika tupi nikala kwa chikulupi mkati mwa Mwana wa Mlungu, uyo wadanikonda ni wadajichocha kwa chifuko changa. 21Siniukana mwawi wa Mulungu, chifuko ngati zene idalipo kupitila lamulo, basi Mpulumusi wadakala wafa chabe.

Chapter 3

1Agalatia owewela, ni diso lanji loipa ilo lawangana? Bwanji Yesu Kristo siwadalangizidwe ngati ozunjidwa pachogolo pa maso yanu? 2Ine nifuna kujiwa ili kuchokela kwanu. Bwa, mdaulandila mzimu kwa vichito va thauko kapena kwa kuvomela chijha mdachivela? 3Bwa , anyaimwe ni vilekwa anthundu uu? Bwa, mudayamba pakati pa mzimu kuti mumalize pakati pa thupi?4Bwa mudazunjika kwa vinthu vambili chajhe ngati ene yadali yachajhe? 5Bwa iye wachocha mzimu kwanu ndi kuchita vichito va mphavu pakati panu kuchita kwa vichito va thauko kapena kwakuvela pamojhi ndi chikhulupi?6Abraham, "wadamvomela Mulungu wadawalengedwa kuti mwene haki." 7Kwa mtundu umweujha jhiwani kuti, wajha avomela ni wana wa Abraham. 8Malembo yadalosa kuti Mulungu wadakawelengela haki wanthu amaiko kwa njila ya chikhulupi. Ulaliki udalalikidwa poyamba kwa Abraham:pakati pa iwe Maiko yonche siyapachidwe mwawi. 9Kuti pambuyo anyiwajha ali ndi chikhulupi apachidwe mwawi pamojhi ndi Abrahamu, uyowadali ndi chikulupi.10Anyiwajha akhulupalila vichito va thauko kwao panchi pa chileso. Pakuti yelembedwa, "waleswedwa kila munthu siwagwilana ndi vinthu vonche valembedwa pakati pa chitabu cha thauko, kuyachita yonche." 11Chipano ni zene kutu Mulungu siwamuwelengela haki ata mmojhi kwa thauko, pakuti mwene haki siwalame kwa chikulupi. 12Sheria siichokana ndi chikhulupi, nampho pambuyo pake, "iye wachita vinthu ivi pakati pa thauko, siwalame kwa thauko."13Kristo wadatiombola ife kuchoka pakati pa chileso cha thauko nyengo iyowadachitika chileso kwa chifuko chathu. Pakuti walembedwa, "waleswedwa kila munthu wahangaika pakati pa ntengo." 14Maganizo yanga yadali kuti, mwawi woudali kwa Ibrahimu udakajha kwawanthu amaiko pakati pa Kristo Yesu, kuti tikhoze kulandila chilango cha Mzimu kupitila chikhulupi.15Abale, nikamba kwa mtundu wa binadamu, ata nyengo malailano ya kibinadamu lathoikidwa chiimile. Palibe uyowakhoza kuudelela kapena kuongezela. 16Chipano ahadi zidakambidwa kwa Ibrahim. Ndi kwa ubazi wake, siwaikamba, "kwa ubazi," kwa mate ambili, popande pambuyo pake kwa mmojhi yokha, "ka ubazi wako," iye ni Kristo.17Chipano nikamba chimwe. Thauko ilolidajha vyaka 430 pambuyo, sichocha malailidwe ya mmbuyo yadaikidwa ndi Mulungu. 18Pakuti ngati kusiidwila kudakajha kwa njila ya thauko, siudakakhancho wajha kwa njila ya ahadi. Nampho Mulungu wauchocha chajhe kwa Ibrahimu kwa njila ya ahadi.19Ndande yanji chipano thauko lidachochedwa? Idaongezeka kwa chifuko cha volakwa, hadi ubazi wa Ibrahimu ujhe kwa anyiwajha kwao adali adanihiwa. Thauko lidaikidwa pakati pa kuchimikizidwa kupitila angelo kwa janja la kuvanichidwa. 20Chipano ovanichana wali ndi mete kupunda ya munthu mmojhi, popande Mulungu ni mojhi yokha.21Kwa chimwecho thauko lilikumbuyo kwa chilanga cha Mulungu? La hasha! Pakuti ngati hauko ilo lidachochedwa lidali ndi uwezo upeleka umoyo, haki idakaphezekana kwa thauko. 22Nampho pambuyo pake, malembo yamanga vinthu vonche panchi pa machimo. Mulungu wadachita chimwe kuti chilanga chakecha kutilamicha ife kwa chikulupi pakati pa Yesu Kristo ikhoze kupatikana kwa wajha akulupalila.23Nampho kabla ya chikulupi pakati pa Kristo siidajhe, tidamangidwa ndi kukhala panchi pa thauko mbaka kujhe kuvunukuidwa kwa chikhulupi. 24Kwa chimwecho thauko lidachitika ochogoza wanthu mbakana Kristo yapowadajha, kuti tiwelengedwele haki kwa chikhulupi. 25Chipano pakuti chikhulupi chafika, tilibeko panchi pa openyelela. 26Pakuti anyaimwe mwaonche ni wana Amulungu kupitila chikhulupi pakati pa Kristo Yesu.27Mwaonche yao mudabatizidwa pakati pa Kristo mwajhiveka Kristo. 28Popande Muyahudi kapena Muyunani, Kapolo kapena olekeleledwa, wammuna kapena wamkazi, pakuti anyaimwe mwaonche ni mmojhi pakati pa Kristo Yesu. 29Ngati anyaimwe ni Akristo, basi ni ubazi wa Ibrahimu, osiidwila kwa mujibu wa chilango.

Chapter 4

1Nikamba kuti malinga osiidwila ni mwana wa libe tofauti ndi mtumik wa chuma chonde. 2Pambuyo pake, waliko phanchipa ophenyeleledwa ndo ozamini mpaka nthawi liyowaikidwa ndibaba wake.3Ndipamenepo ndi ife, yapotidali wana, tidagwilidwa kupitila utumwa wakanun zapoyamba za pajhiko. 4Nampho nthawi yabwino yapoidafika, Mulungu wadamtuma mwana wake, obadwa ni wamkazi, obadwa phanchi palamulo. 5Wadachita chimwecho ili kuwalamicha anyiwajha adali phanchi palamulo, ili kuti tulandile hali ya kuti ngati wana.6Kwachifuko anyaimwe niwana, Amulungu wadamtuma roho ya mwana wake mkati mwa mitima watha, Roho watana, "Abba, Baba." 7Kwa chifuko ili iwe osati kapolonche ila mwanangati ni mwana, basi iwe naweosidwila kupitila Mulungu.8Ata kabla nthawi siwadamjiwe Mulungu,mdali akapolo kwa anyiwaja ambao kwa asili ndi osati vosepa kabisa. 9Nampho chipano kuti mumjiwa Mulungu, au kuti mjiwika ndi Mulungu, ndande yanji mbwelancho kukanuni dhaifu zaoyamba ndi zilibe za mate bwa? Mfuna kukalancho akapolo ncho?10Mzigwia kozipenyelela siku maalumu, mandamo ya mezi, majina ndi vyaka ndiopa kwa chifuko chanu. 11Niopha kuti kwa chinthu fulani, najiangaisha chabe.12Nikutondozani, abale, mkale ngati umonili, kwa chifuko nili ngati umonili. Simdanilakwile. 13Nampho mjiwa kuti idali ni kwa chifuko cha utenda wa tuphi kuti nilinena mau kwanu kwa nyengo yoyamba. 14Ingakale hali yanga ya mtuphi idakuikani kupitila maeso simdandizarau au kunikana, pambuyo pake mdanilandila ngati angelo wa Mulungu, kana kuti nidali Kristo Yesu mwene.15Kwa chimwecho, chilikuti chiphano chisangalalo chanu? Pakuti nishuhudia kwanu kuti ikakozekana, mdanalizuia maso yanu ndi kunipacha ine. 16Chimwecho chiphano, bwa mdani wanu kwachifuko nikukambilani uzene?17Akufunanifunani kwa mbwembwe, nampho osati kwa vabwino, afuna kwalekanicha anyaimwe ndiine ili mwachate. 18Ni bwino kukhala ndi hamuchifuko zili za bwino, ndi nthawi yaponikhala pamojhi namwe.19Wana wanga wang'ono nidwala uchungu kwa chifuko chanu tena mpaka Kristo waumbidwe mkhati mwantu. 20Nidakhakonda kukhalapo pamojhi namwe chipano ndi kung'anamula sauti yanga, kwa chifuko ndili mantha pakati panu.21Nikambile anyaimwe ambao mkumbila kukala panchi pa lamulo umolikhambila. 22Pakuti yalembedwa kuti Abrahamu wadali ndi wana wachimuna awili, mmojhi kwa yujha wamkazi kapolo ndi mwina kwa wamkazi osililidwa. 23Ata chimwecho, yujha wakapolo wadabadwa kwa nthupi tu, nampho yujha wamkazi osililidwa wadabadwa kwa ahadi.24Vinthu ivi vikoza kukambilidwa kwa kutumia mfano, pakuti wachikazi anyiyawa alingana ndi ogwilizana awili, mmoji wao kuchokela kupitila phili kubadwa wana ambao ndi akapolo, uyu ni Hajiri. 25Chipano Hajira ni phili Sinai uliko Kuarabuni, lilinganichidwa ndi Kuyerusalemu ya chiphano, pakuti ni kapolo pamoji ndi wana wake.26Nampho Yerusalemu ambayo ili kumwamba ni dangalila, ndi ii nde mama wathu. 27Pakuti yalembedwa, "sangalala, iwe wamkazi uli osabule, iwe siubala, kuweza sauti ndi uthimbe kelele kwa chisangalalo,iwe ambae ulibe uzoefu wa kubala. Kwa ndande ambili ni wana wa auyowali mgumba, zaidi ya wajha ayujha ambae wali ni wammuna."28Chiphano, abale ngati Isaka, namwe ni wana wa ahadi. 29Kwa nyengo ijha ambapo munthu yujha wadabadwa kwa mujibu wa mzimu wa chiphano ni chimchijha.30Malembo yakamba bwanji? "Mumchoche wamkazi kapolo pamoji ndi mwana wake wa mmuna pakuti mwana wamkazi kapolo siwasiidwile pamoji mwana wamkazi osililidwa." 31Kwa chimwecho, abale ife osati wana wamkazi kapolo, naphoni wa mkazi osililidwa.

Chapter 5

1Ni kwa ndande Kristo adatipacha ufuru, mmwemo imani molimbikila wala msadakodwancho mwa Luzi la akapolo. 2Penyani ine Paulo, nikukambilani kuti mkakala mwaumbalidwa, Kristo siwakupindulani kwa njila yaliyonche ijha.3Tena nimlalikila kila wamuna uyowaumbalichidwa kuti wafuika kulimbikila kwa matauko yonche. 4Mwapatulidwa kwa kutali ndi Kristo, anyiwaja wonche mwehengedwa malinga kwa matauko. Mwagwa kwakutali ndi mawi.5Kwa mate kwa njila ya Mzimu, kwa chikulupi tiyembekeza mbhavu ya malinga. 6Mwa Kristo Yesu kuambalichidwa kapena osati kuumbalichidwa palibe mate yaiyonche. Ndi chikulupi choka chichita nchito kupitila chikondi ndicho chilangiza chindhu. 7Mdali ndimbula liwilo bwino. Yani wadakuchekelezani oavechele zene? 8Kunyenga kwa kuchita chimwecho sikuchoka ka iye wakutanani anyiimwe.9Kulujhuka pang'ono kuwananga donge la mphumphu. 10Ndili ndi chikulup ndi anyiimwe mwa Ambuye kutisimganizila kwa njila yena yaliyonche. Waliyenche yujha siwakusowecheni siwabale lamulo lake iye mene waliyenche yujha.11Abale ngati niendekela kulalika jando kwa chifukochiyani nikali kuvutichidwa? Kwa nkani iyi chujha, chochekeleza cha mtanda sichikoze kuwanangidwa. 12Ndi chifuko changa kuti anyiwajha wachogolela kuyipa siwajiwnange achinawene.13Mulungu wakutanani anyiimwe, abale, muyu ufuru. Ikanda msaada uchitila ufuru wanu ngati chinamizilo cha tupi pamalo pake kwa chikondi mtangatilane anyiimwe kwa anyiimwe. 14Pakuti matauko yonche yakwanilichidwa kwa tauko limojhi: nayo ndi, "ndi mditu umkonde wapafupi pako ngati wamwene wake." 15Nampo ngati nkalumana ndi kudyana, jhipenyeni kuti msadajhiwananga anyiimwe kwa anyiimwe.16Ndi nena, yendani kwa mzimu, ndipo simzikwanilicha kumbilo la tupi. 17Pakuti tupi lilindikukumbila kwakukulu kupunda mzimu, ndi mzimu uliokumbila kwa kukulu kupunda tupi. Izi zichuchana kila mmojhi ndi yena.Yochokela ndi kuti simchita vindhu mkumbila kuvichita. 18Nampho ngati mzimu ukuchogozani anyiimwe, simli panchi pa matauko.19Chipano vochita va tupi vionekana. Nayo ndi chiwelewele, ukaalili, ufisadi, 20kupembhela chosepa, ufiti, udani, ndeo, kupenya kuipa, kukwelela mphayi, kupiisana, kuyambana, kudulana kwa madhehebu. 21Nchanje, kulojhela ludyo, ndi yochita yena ngati yaya. Nikuyaluzani anyiimwe ngati umonidakuyaluzani mmayambo kuti anyiwajha achita vichito ngati ivi siasidwila ufumu wa Mulungu.22Nampho chipacho cha MZimu ndi chikondi, chimwemwe mtendele, kudikila, kuchocha, kuchita vabwino, chikulupi. 23Upole ndi pang'ono. Palibe tauko kupita vichito ivi. 24Anyiwajha aliwa Kristo Yesu aliwamba tupi pamojhi ndi maganizo ndi kukumbils kwawo kuipa.25Ngati sitilame kwa Mzimu, naponcho sitinale kwa Mzimu. 26Sitidakala ndi dama sitidayambana kila mmojhi ndi mnjake, kama tidaonekalana nchanje.

Chapter 6

1Abale wanga, munthu wakalakwila, anyiimwe muli amzimu m'bwezeni munthuyo wajikonje bwino, ndi mjipenyelele mngalowe mmayeso ya ndani. 2Tengelanani makatundu, kwa icho simkwaniliche tauko la Kristo.3Ikakala munthu walionje wajiona waliwa bwino ni nyengo osati kanthu, wjainyenga mwene. 4Kila munthu waliyese nchito yake nde yapo siwakale ndi ndande yojielekela iye mwenepe osti ndi kwa anjake. 5Mateyake kila mmoji siwatenge bandulo lake mwene.6Opunzila wamkambila vabwino vonche mpuzisi wake. 7Msanyengeka, Mlungu samchitila mphwasanje icho wavyala munthu nde icho siwagoole. 8Mateyake uyo wavyala kwa tupi lake kumbilo la jiko la panchi, siwagoole zowangika za mjiko la panchi, nampho wakavyala mwa Mzimu, mwa mzimuyo siwagoole moyo wa muyaya.9Kenaka tisadalema kuchita vabwino, mateyake sitigo ole panyengo yake ngati mitima yatu siikomoka. 10Kwa icho umotipatila malo taachitile vabwino wanthu onche nditu anyiwaja akulupitila.11Penyani umo nikulembelani kwa malembo yayakulu ndi kwa janja langa namwene. 12Onche afuna kuonekana abwino kwa vinthu vatupi nde yao akuchisani kuumbalidwa, kuti sadaipichidwa ndande ya mtanda wa Kristo, chimwechope. 13Mate yake ingakale anyiiwo aumbalidwa sagwi la tauko, afuna anyiimwe muumbalidwe ajione alibwino kwa matupi yanu.14Nampho sinikoza kujidama kwa chinthu chilichonche, koma mtanda wa Ambuye watu Yesu Kristo mwa umeneo jiko la panchi kwambidwa kwaine ndi ie kwa jiko la panchi. 15Ndande kuumbalidw osati kanhu ndi osaumbalidwe osati kantu, nampho chilengedwe cha chapano. 16Onche yao saakale mu ukalo uumtendele ukale kwa ndi kulekelela, kwa Israeli wa Mlungu.17Kuyambila chapano munthu wasanivuticha, mate yake nitenga mthupi mwanga. 18Abale wanga, mwawi wa Ambuye watu Yesu Kristo ndi ukale pamoji ndi mizimu yanu. Amina.

Ephesians

Chapter 1

1Paulo kapolo wa Kristo Yesu kwa chikondi cha Mulungu, kwanyizawa aikidwa pamphepete kwa chifukwa cha Mulungu ali Kuefeso ndi anyiyawa okulupalika kupitila Kristo Yesu. 2Mwawi ukale kwanu ndi mtendele uwouchoka kwa Mulungu tate wanthu ndi mbuye Yesu Kristo.3Mulungu ndi tate wa mbuye wanthu Yesu Kristo waninkhidwe sifa. Ndiiye watibariki kwa kila baraka za kimizimu, kupitila malo ya mwamba mkati mwa Kristo. 4Kabla ya malengedwe ya jhiko, Mulungu wadatusankhula ife ambaa tukulupalila kupitila Kristo wadatusankhula ife ili tukoze kukala oyela ndi sitilaumidwa pachogolo pake.5Kupitila chikandi cha Mulungu wasatusankhula mmayambo kwa kututenga ngati wana wake kwa njila ya Yesu Kristo wadachita mchimwechi kwa chifukwa wadakondwelezedwa kuchita chija ichawadakhumbila. 6Matokeo yake ndi kuti Mulungu watukuzidwa kwa mwawi chitukuka chake ichi ndeicha wtuninkha bure kwa njila ya okondedwa wake.7Pakuti kupitila okodedwa wake, tulamichidwa kupitila mwazi wake, kurekeleledwa kwa vachimo tulinalo ili kwachifukwa cha ufuluwa mwawi wake. 8Wadachita mwawi uu kukala wambili kwa chifukwa chathu kupitila ulemu wa njeru.9Mulungu wadachita ijuike kwathu ujo uzene uoudabisika wa mpango, kupitila njeru idaonekana mkati mwa Kristo. 10Nyengo ntawi zakuwanila kwa kukwanila, kwa mpango wake, Mulungu siwaviike pamoji kila chinthu cha kumwamba ndi chapamwamba pa kujhika mkati mwa Kristo.11Kupitila Kristo tudasankhulidwakwa dala kabla ya nyengo ii idali ndi kupitilandi mpano wa uyo wachita vinthu vonche kwa dala la chikondi chake. 12Mulungu wadachita mchimwecho ili kuti tukoze kuchalapo kwa sifa ya chitukuka chake, tudali oyamba kukala ndi ujasili mkati mwa Kristo.13Idali kwa njila yaKristo kuti mdavela mau la uzene, utenga wa Mulungu wa kulamichidwa kwanu kwa njila yaKristo idali kupitila iyencho kuti mwakhulupalla ndi kutilidwa chidindo cha Mzimu Oyela uyowaaididwa. 14Mzimu ndo adhamini kwa kusiidwila kwanthu mpaka lamula yapasilipatikane ii idali ndi kwa sifa ya chitukuka chake.15Kwa chifukwa ichi, tanu nyengo ndidavela kuhusu chikulupi chanu mkati mbuye Yesu ndi kuhusu chikondi chanu kwa anyiwaja onche ambao aikidwa pamphepete kwa chifukwa chako. 16Sindida sie kumyamikila Mulungu kwa chifukwa chanu ndi kwaataja kupitila mapemphelo yanga.17Ndipempha kuti Mulungu wambuye wathu Yesu Kristo, tatewa chitukuka, siwa kuninkheni mzimu wa ulemu, kuchakula kwa njeru zake. 18Ndipempha kuti masa yanu ya mmitima ya tiridwe dangalila kwa anyiimwe kujiwa ndi uti ujasiri wa kutanidwa kwanu. Ndipempha mjiwe ufulu wa chitukuko cha siidwi la kwake mkati mwa anyiwaja aikidwa pamphepete kwa chifukwa chake.19Ndipempha kuti ajiwe uulu upunda mphavu ya mkatimwathu ambao tukhulupalila uu ukulu ndi kupitila ndi kuchita kupitilamphavu zake. 20Ii ndi mphavu iyoyachita nchitomkati mwa Kristo nyengo Mulungu yapo wadamhyusha kuchoka kwa akufa ndi kumkazika kupitila janja lake la kuchimuna kupitila malo ya kumwamba. 21Wadamkazika Kristo pamwamba patari ndi kutawala lamulo, mphavu enzi ndi kila jina ilolitajidwa, wadamkazika Yesu asatipe kwa nyengo ii nampho nyengo ikujancho.22Mulungu wa vichita vinthu vonche panchi pamyendo ya Kristo. Wamchita iye munthu pamwamba pa vinthu vonche kupitila nyumba ya mapemphelo. 23Ndi nyumba ya mapemphelo kuti nde thupi lake, kukamilika kwake uka kujaza vinthu vonche kupitila njila zonche.

Chapter 2

1Ngati vija kuti mafa pakati pachimwa ndi zambi zanu. 2Idali pakati pa yaya kuti kwaza mdapita kulingana ndindawi zajiko lino. Mdali ndiapita kochata kuchogoza ndi mamlaka ya kumwama iyi nde umoyo wake yuja wachita njito pakati pawana wa achimwa. 3Ife taonje pakaletidali mmalo wa yawa savananavo tidali ndi tichita pandende la kukumbila kuipa ka patupi patu. Tidali nitichita zofuna zatupi ndi zelu zatu. Tidali kwa chisisi wana apwai ngati wina.4Nambo Mulungu ndiwambili wodalisa pandande yachikondi chake chachikulu ilowadatikondela ife. 5Ndawi tidali akufa polakwa kwatu, adatipeleka pamoji pakulama kwa nyuwa ni mkati mwa Kristo ndepachikondi kuti machilisidwa. 6Mulungu wadatiucha pamoji ndi kutichita kukala pamoji pamalo pamalo pajiko mkati mwa Kristo Yesu. 7Wadachita ichi ili pakutipa ndawi zibwela wakoze kutilangiza kulemela kwakulu pa mtendele wake kutilangiza ife panjila yabwino wake mkati mwa Kristo Yesu.8Pachimwemwe machilisidwa panjila yachikondi ndiiyi sidachoke kwatu ndi mbaso ya Mulungu. 9Sichokana ndi vindu chochitika chake, wasidakala mmoji wake ojielekela. 10Pandande ife tilimunjito ya Mulungu, taengedwa pakati pa Kristo Yesu kuchita vindu vabwino. Ndivichito ivi yayo Mulungu wadalenga choka pakale pandande yatu, ilitiende pakati payayo.11Pachocho kuti pakale mudali wandu amjiko pandande yatupi mwitanidwa, "simuli nditoala" pachija chitanidwa toala latupi iyoichitidwa kwa manja ya wandu. 12Pandawi imene mudali osangidwa ndi Kristo mudali alendo paagano la ahadi simudali ndi vauzene wandawi ibwela mudali owina pakati pajiko.13Nambo chapano pa Kristo Kristo anyiimwe muli pakalepo mudali kutali ndi Mulungu mapelekedwa pafupi ndi Mulungu pamwazi wa Kristo. 14Pakuti iye ndemtendele watu wadachita viwili kukala chimoji. Patupi lake wadali wananga pupa kosangana kuli watusianicha, umene udani. 15Kuti waakomecha malamulo ya msanga ndi kanuni ilikuti walenge mundu mmoji wanyuwani mkati mwake. Wakachite mtendele. 16Wadachita ichi ili kwakanichana makundi yawili yawandu kukala awii mmoji kwa Mulungu kupitila pamusalaba, panjila ya msalaba wadaubisa udani.17Yesu wadaja ndi kulalika mtendele kwanu anyiimwe mudali kutali ndi mtendele kwao waja adali pafupi. 18Pakuti panjilaya Yesu ife taonje awili tili ndi nafasi kwa yujha Roho mmoji kulowa kwa Atate.19Chocho basi anyiimwe wandu wa mjiko opande oyenda walendo njo. Bali muli machinawene pamoji ndi waja adasiidwa panjila ya Mulungu ndi ajumbe panyumba ya Mulungu. 20Mamangidwa pamwamba pa msingi wa otumidwa ndi olosa. Kristo Yesu mwene wadali mwala waukulu la pambepete. 21Pakati paiye nyumba yonje lalinganichidwa pamoji kukala ngati kanisa mkati mwa Mbuye. 22Ndi mnyumba yake imwe namwe mmangidwa pamoji ngati pamalo polama pa Mulungu pakati pa Roho.

Chapter 3

1Kwa ndande ya ili ine, Paulo ni omangidwa wa Yesu Kristo kwa chifuko chnu mataifa. 2Ni khulupilila yakuti mwavela pakati pa nchito ya mwawi wa Mulungu uwowanipacha kwa chifuko chanu.3Nikulembelani kuchokana ndi kuvunukulidwa umo wavunukudwila kwanga. Uu ni uzene uo udabisika uonidalemba kwa kuchepecha mkalata injake. 4Yapo usoma kukhuza yaya, ukhoza kujhiwa ulemu wanga pakati pa uzene uu uoudabisika kukhuza Kristo. 5Kwa ubazi unjake uzene uu siudachitidwe ujhiwikane kwa wana awanthu. Nampho chipano waikidwa wazi kwa mzimu kwa atumiki yao agawika ndi olosa.6Uzene uu udabisika ndi kuti wanthu amataifa ni ashiliki anjathu ndi ajumbe anjathu athupi niothangatilana pamojhi ndi ahadi ya Kristo Yesu kupitila ulaliki. 7Ni kwaili nachitika mtumiki kwa zawadi ya mwawi wa Mulungu uowachochedwa kwanga kupitila kuchitika kwa mphavu yake.8Mulungu wadachocha zaadi ii kwanga, ata ngati ine nimunthu wa mng'ono kwa onche pakati pa onche yao adapatulidwa kwa chifuko cha Mulungu. Zawadi ii nikuti inifuna kwa thangatila amataifa ulaliki wene uo siufunidwa funidwa wa Kristo. 9Inifuna kwamulikila watu onche pakati pa chyani ndi chifuno cha Mulungu wa chisisi. Ichi ni chifuno uoudabisidwa kwa vyaka vambili ivovapita, ndi Mulungu uyowadviumba vinthu vonche.10Ii idali kuti, kupitila kanisa, achogoza ndi mamlaka pakati pa malo ya kumwamba apate kujhiwa nchonga za mbili asili ya ulemu wa Mulungu. 11Yaya yadakachokela kupitila mpango wa muyaya uo udaumalizila mkati ma Kristo Yesu Ambuye wathu.12Pakuti pakati pa Kristo tili ndi ujasili ndi kukhoza kulowa kwa ujasili kwa chifuko cha chikulupi chathu kwaiye. 13Kwa chimwecho nikupemphani msidadula khumbilo kwa chifuko cha mavuto yanga kwa ndande yanu yaya ni ufulu wanu.14Kwa ndande ii nigwada kwa Atate. 15Uyo kwa iye kila familiya kumwamba ndi pamwamba pa jhiko watanidwa jhina. 16Nipempha kuti apatye kuwanemecha, kuchokana ndi ulemelelo ndi ufulu wake wachite chiimile kwa mphavu kupitila mzimu wake uwo uli mkati mwanu.17Nipempha kuti Kristo walame mkati mwa mitima yanu kupitila chikhulupi. 18Nipempha kuti mukhale ndishina ndi msingi wa chikondano chake. Mukale pakati pa chikondi chake kutimukhoze kujhiwa, pamojhi ndi onche avomela, jinsi ikulu, ndi utali ndi msinkhu ndi kina cha chikondi cha Kristo. 19Nipempha kuti mjiwe ukulu wa chikondi cha Kristo, uo upitilia kujhiwa muchite yaya kuti mujazidwe ndi kuenela konche kwa Mulungu. 20Ndi saino kwaiye wakhoza kuchita kila chinthu kupunda kwa yonche yayotiyapempha kapena yayotiganiza, kupitila mphavu yake ichita nchito mkati mwathu. 21Kwa iye kukhale ufulu mkati mwa kanisa ndi pakati pa Kristo Yesu kwa ubazi onche muyaya ndi muyaya.Amina.

Chapter 4

1Kwaicho, ngati omangidwa ndande ya Ambuye, ndikupemphani mjienda oyenela ngati umo Mlungu wadakutanitani. 2Mjikala ojichepecha ndi ofasa ndi kulimba mtima ndi kutengelana mkati mwachikondi. 3Sungani umoji wa Mzimu Oyera pa mtendele.4Pali thupi limoji ndi Mzimu Oyela umoji, ngati umomudatanidwila ndiposo ndiponso pali chiyembekezo chimoji icho Mlungu wadakutanilani. 5Ndi pali mbuye mmoji, chikuluparilo chimoji, ndi ubatizo umoji. 6Ndi Mulungu mmoji atate awanthu wonche. Iye wali pamwamba pa vonche, ndi yonche ndi mkati mwayonche.7Waliyonche waife wapachidwa mphaso yake molingana ndi Kristo mmene wamaperekera mphaso zake. 8Ngati malembo umo yakambila, yapowadakwela kumwamba mwamba wadachogoza gulu la akapolo, ndikugawira wanthu mphaso.9Nde chiyani mate ya mau, "wadakwela" ikapanda kuti wadacheka panchi? 10Uyo wadachika ndi munthu mweyuja uyo wadakwela kumwamba konche. Wadachita izi kuti wajiwika pa vinthu vonche.11Kristo wadachocha mphaso ngati izi, mtumiki, , Aneneri, Alaliki, Abusa ndi Amphumisi. 12Wadachita izi kuti wanthu Amlungu akozere tu kuti akagwire nchito yotumikila, ndande ya kumanga thupi la Kristu. 13Wachita izi makana ife tifikile pa umoji wa chikulupililo ndi malango ya mwana wa Mlungu wachita izi mbakana tikwime ngati anyiwaja ndikufika nthundu wa Kristo.14Izi kuti tisakhalancho ngati wana, tisimaponedwa ponyedwa uku ndi uko. Kuti tisatengedwa ndi mtundu wina walionche wa mayaluzo, pa kunyengedwa ndi wanthu ochenjela. 15Pambuyo pake sitikambe uzeni mkati ma chikondi ndi kukula kupunda munjila zonche mkati mwake iye wali nde munthu Kristo. 16Kristo watilumikiza pamoji thupi lonche la ophemphela, lalumikizidwa pamoji ndi chiwalo chalichonche kuti thupi lonche lijikula ndi kujimanga lene mchikondi.17Kwaichi ndikamba izi, ndikupemphani mwa Ambuye: msayendancho ngati wanthu amitundu ya kunja umo aendela ponyengedwa ndi njelu zao. 18Atilidwa mdima mmaganizo yao, atopoledwa kuchoka mu umoyo wa Mlungu pa umbuli uli mkati mwao ndande ya kulimba kwa mitima yao. 19Sajivela manyazi, ajipeleka achinawene wake pa vichito vao voipa, ndi kila mtundi wa kumana.20Nampho simudayaluzidwe chimwechi mkati mwa Kristo. Ndiganiza kuti mwavela za iyeyo ndiganiza kti mwakhala uyaluzidwa za ieyo, ngati umo uli uzene mkati mwa Yesu. 21Ndiganiza kuti mwavela za iyeyo ndiganiza kuti mwakhala uyaluzidwa za iyeyo, ngati umo uli uzene mkati mwa Yesu. 22Mfunika kuvula vichito vichatana ndi maendedwe yanu ya kale, umunthu wa Kale ndiumunthu wa kale uola chifukwa cha kumbilo la unami.23Vulani umunthu wanu wa kale kuti mchitie achiphano mkati mwa mzimu wa njelu zanu. 24Chitani chimwechi kuti mkozekuvale umunthu wa chipano, wafanana ndi Mlungu woumbidwa ndi chilungamo ndi kuyera mtima.25Kwaicho unami uikeni patali. Kambani uzene kila munthu ndi mnjake, pakuti tigwilizana mmoji ndi mnjake. 26Khalani ndi mphwayi nampho msachita machimo lisabila zuwa mkali ndi mphwayi zanu. 27Satana musamphacha malo.28Wakuba waliyonche wasabencho. Pambuyo pake wajigwila nchito. Pa manja yake wajigwila nchito ya chilungamo, kuti wakhoze kumtandiza munthu osowedwa. 29Mau yoipa yasachoka mkamwa mwanu, pambuyo pake mau ya bwino yajichoka mkamwa mwanu, kwapacha pindu yawe avela. 30Ndi msaudandaulicha Mzimu Oyera wa Mulungu, kwaiye kuti mwadindidwa chidindo chifukwa cha tsiku lija la upulumuchidwa.31Ikani patali kuwawa konche,mphwayi, ndeo ndi mau ya chipongwe pamoji ndi kuipa konche, kalani okondana anyaimwe kwa anyaimwe. 32Mkale alisungu, mjikululukilana mwachinawene kwa mwachinawene, ngati mujha Mulungu mkati mwa Kristo umo wadakukuhulukilani anyaimwe.

Chapter 5

1Kwa icho mukale wandhu wa kumchata Mlungu, ngati wana waiye okondedwa. 2Muyende mwa chikondi, mmwemujha ngati Kristo umo wadatikondela ife wadajhichocha mwene kwa chifuko chatu. Iye wadali nchembe ndikukoleza kukhala kunungila kwa bwino kwa kumkondolyecha Mulungu.3Chigololo kapena ukadili waliwonche ndi kukumbila kuipa lazima visitatajhidwa pakati panu, ngati imoifunikila kwa anyiyawo akulupalila. 4Wala iyoipicha yasadatajhihidwa, mau ya kipumbavu, kapena michetu ya kutukwana, yayo osati ya bwino, pambuyo pake pakale kuyamikila.5Mkoza kukala ndi chilinga cha kuti kuli chigololo, ukadili, kapena okombila. Mmeneyo ndi wakukambila chospa walibe kusidwila kwa chalichonche mwa ufumu wa Kristo ndi Mulungu. 6Mundhu waliyenche asakunyenga kwa mau yoka; kwa nande vichito vimenevo mbwayi ya Mulungu ikujha pa mwamba pa wana okana. 7Mmwemo usadagwilizana pamojhi ndiamjiwo.8Pakuti anyiimwe mmayambo mdali mdima, nampho chipano muli adangatila mwa Ambuye. Mmwemo yendani ngati wana wa adangalila. 9Pakuti vipacho vadangalila vijhumushidwa kukadwa konche, malinga ndi zene. 10Funa chijha chikondolecha kwa Ambuye. 11Usadakalapo ugwilizano mwa nchito za mdima zosesi ndi vipacho, pambuyo pake zikidwe poyera. 12Kwa ndande machitidwe yachitidwa ndi anyiiwo mobisika ndi nchoni kupunda ata kuyakambilila.13Yochita yonche, yapoyavunukulidwa ndi dangalila, yakala wazi. 14Pakuti kila chinthu ichochavumbulidwa chikala mdangalila. Mmwemo anane chimwe, "Uka, iwe wagona, ndi ima kuchokela kwa akufa ndi Kristo siwamulikile pamwamba pako."15Mmwemo mkale ojipenyelela umo muyendela, osati ngati wandhu opande kujhwa akapunda ngati ojhiwa. 16Ipulumucheni ntawi pakuti siku ndi zoipa. 17Msadakala osasome pambuyo pake jhiwani chiyani chinondi cha Ambuye.18Msadalojhela kwa mvinyo uchogoza kuwananga, pambuyo pake mjazidwe ndi Mzimu Oyela. 19Kambani ndi ila mmojhi wanyiimwe kwa Zaburi, ndichiyelekelo, ndi nyimbo za mumtima. Imbanindi yelekelani kwa mtima wa Ambuye. 20Nyengo zonche chocha mayamiko kwa vinthu vonche mwa jhina la Kristo Yesu Ambuye watu kwa Mulungu Atate. 21Jhichocheni mwachinawne kila mmojhi kwa mwena kwa ulemu wa Kristo. 22Wachikazi, jhichocheni kwa wachimwena wanu, ngati kwa Ambuye. 23Kwa ndande wanuena ndi mutu wa mkazi ngati Kristo umu wali mutu wa kanisa, ndi chiombololo cha tupi. 24Nampho ngati kanisa umolilipanchi pa Kristo mmwemo wachikazi nditu achite chmwecho kwawachimuna wao mwa kila kamtu.25Wachimuna okondeni ochakazanu ngati mujha Kristo umowadalikondela kanisa ndi wadajhichocha mwene kwa chifuko chake. 26Wadachita chimwecho kuti likale logela. Wadalichana kwa kuliyelecha ndi majhi mwa mau. 27Wadachita chimwechi kuti akoze kujhipelekela mwene kanisa kuyela. Popande ndi mdolio kapena waakapena chinthu chifanana ndi yaya pambuyo pake ndi kuyela lopande ndi kulkwila.28Kwa njila imweijhe wachimuna mfunika kwakonda achakazao ngati matuphi yawo. Yujha wamkondea mazake wake wajhikonda mwene. 29Palibe ata mmojhi watenga tupi lake. Pambuyo pake, waupachetanzi di kuukonda ngati Kristo nayencho umo wadalikondela kanisa. 30Pakuti ife ndi wachigwilano wa tupi haiye.31Kwa ndande iyi wammuna siwamsiye toto wake ndi mayi wake ndi kulunjana ndi mkazi wake, ndi achameneo awili siakale tupi limojhi. 32Uwu udali wabisika. Nampho ninena kukuza Kristo ndi kanisa. 33Nampho kila limojhi wanu ndite wamkonde mkazake ngati mwene ndi mkazi nditu amlemekeze mmunake.

Chapter 6

13Wana lemekezani obala wanu mwa Ambuye mate ndi malinga. 2Lemekeza atate wako ndi amai wako (limenendi lamlo loyamba lili ndi lonjezo). Kuti upeze masiku yambili pa jiko la panchi.4Namwe anyaatate msaayamba achiwana wanu koma aleleni mwa ulemu ndi mayaluzo ya Ambuye.5Akapolo lemekezeni mabwana wanu apano pajiko la panchi , kwa mantha ndi kutenthemela kwa mtima wa bwino ngati mumlemekeza Kristo. 6Osati kwa ukapolo wa masope ngati yao ajikondelecha kwa wanthu, koma ngati akapolo Akristo, ndi mchita kwa mtimawa bwino vimkondelecha Mlungu. 7Kwa mafuno yabwino ngati kumtukila Ambuye osati wanthu. 8Ndi mjiwa kuti kila mau la bwino ilo wachita munthu siwapachidwe limwelo ndi Ambuye wakale kapolo kapena fulu.9Namwe Mabwana achitileni anyiiwo chimwecho popanda kuaofya, ndi mjiwa kuti wali mbuye wao ndi wani wali kumwamba, kwa iye kulibe kukonda akumoji.10Endekelani kukala olimbikila mwa Ambuye mwachikozelo cha mphavu zake. 11Valani zida zonche za Mlungu mkoze kukangana ndi satana.12Mateyake nkhondo yatu osati ya mwazi ndi nyama koma ulamulo wa fumu ndi wankulu amdima ndi asrikali a mizipo yoipa pajio la panchi la mizimu. 13Kwa icho valani zida zonche za Mlungu, kutimkoze kupikisana pa siku lija likafika ndi mkato kwanilicha yonche, muime chiimile.14Kwa icho imani kuno mwavala uzene mchiono ndi malinga pa chidale. 15Ndi kumbilo lo lalika utenga wa bwino likale ngati sapato mmyendo mwanu. 16Vonche vonche valani chilindo cha chikulupi, siikukozecheni kutima nthungo za ndani.17Valani chisoti cha chipulumuso ndi chikwanje cha mzimu, nde mau la Mlungu. 18Pamoji ndi mapemphelo, pemphani kwa mzimu kila nyengo, jipenyeleleni kila nyengo ndi udikililo onche ndi mapemphelo kwa okulupilila onche.19Pemphani kwa ndande yanga kuti nipachidwe utenga yapo nimasula mlomo wanga. Pemphani kuti nikambe kwa mphavu zene yabisika mu utenga. 20Ndande ya utenga ine ndi mtenga namangidwa vingwe kuti mkati mwao nikambe kwa mphavu umo ifunikila.21Nampho anyiimwe mjiwe vinthu vanga ndi umoniendekela, Tikiko m'bale wana okondeka ndi mtumiki okulupilika mwa Ambuye, siwakujiwicheni kila kanthu. 22Namtuma kwanu kwa ndande iyi, kuti mjiwe vinthu vitikuza ife, wakoze kukondwelecha mitima yanu.23Mtendele ukale kwa abale ndi chikondi pamoji ndi chikulupi kuchoka kwa Atate Mlungu ndi Ambuye Yesu Kristo. 24Mwai ukale pamoji ndi onche amkonda Ambuye Yesu Kristo kwa chikondi chija chosafa.

Philippians

Chapter 1

1Paulo ndi Timotheo, atumiki a Kristo Yesu kwa waja adapatulidwa mwa Kristo akala Kufilipi, pamoji ndi apenyelela ndi madikani. 2Lisungu ndi mtendele kuchoka kwa Mulungu atate watu ndi ambuye watu Yesu Kristo.3Nimuyamika Mulungu wanga ujapo nikuku mbukilani mwaonche. 4Nyengo zonche pemphelalanga chifukwa chanu mwaonche nikondwela yapo nikupemphelani. 5Nili ndi mayamiko yambili chifukwa cha mgwilizano wanu mwa mau ya Mulungu Chiyambile siku loyamba mpaka lelo. 6Nikulupilila kuti iye wadanyambika nchito ya bwino ya bwino mkati mwanu siwaendekele kuisiliza mbaka siku ya ambuye Yesu Kristo.7Ni bwino kwa ine kujivela chimwechi kwanu mwaonche ndande nakuikani mumtima mwanga ndande anyiiimwe mwakala ogwili zana ndiine Mulisungu pa kamangidwa kwanga ndi utetezi wanga wa mau la Mulungu. 8Mulungu ndi mboni wanga umo ndili ndi kumbilo kwanu mwa mkati wa chikondi cha ambuye Kristo Yesu.9Ndi nimpempha kuti chikondi chanu chikuluke kupunda mwa malango ndi njelu zonche. 10Nipempha kwa ichi mukale ndi ukozelelo woyesela ndi kusankha vinthu vili vabwino kupunda nikupemphelani mukale woyela popanda mlandu ulionche pa siku ya Kristo. 11Nampho mjalichidwe ndi chipacho cha matechi pezeka mwa Yesu Kristo kwa kuyela ndi uelekelo wa Mulungu.12Chipano abale wanga ndifuna mjiwe kuti vinthu vichokela kwanga vichita mau la Mulungu liendekele kupunda. 13Nde ndande kumangidwa kwanga mwa Kristo mwajiwika mwa openyelela boma onche ndi kwa kila munthu. 14Ndi abale ambili mwa ambuye chifuko cha kumangidwa kwenga apeza kumbilo ndi kufuna kulalika mau popande mantha.15Wina zene aakamba ambuye Kristo kwa nchanje ndi ndeo ndi wina kwa mtima wabwino. 16Yao amkamba Kristo mwa mtima wa bwino ajiwa kuti naikidwa pano ndande yoteteza mau la Mulungu. 17Wina amkamba Kristo mojipatula ndi mtima oipa aganiza kuti andipelekela mavuto mwa maluzi yangu.18Kwa icho siniopa, ikale njila yoipa kapena ya zene Kristo walalikidwa mwa ichi nikodwa yetu sinikondwe. 19Ndande nijiwa kuti ichi sichipeleke kumasulidwa kwanga ichi sichipezeke ndande ya mapemphelo yanu ndi mtandizo wa Mzimu wa Yesu Kristo.20Mwa chikulupi changa cha zene ndikuti sinidaona nchoni pamalo pake mwa mphavu zonche ngati siku zonche ndi chapano mkulupilila kuti Kristo siwakwezedwe mwatupi langa ingakalemwa umoyo kapena mwa nyifa. 21Mate kwa ine kukala ndi Kristo ndi kufa ndi pindu.22Nampho ngati kukala kwa tupi m'bale chipacho mwa nchito yanga mwa icho sinijiwa ndi chili chosanka. 23Mate nditutuzidwa kupunda ndi maganizo yawili yaya, nili ndi kumbilo la kulisia tupi ndi kukala pamoji ndi Kristo, chinthu cha mtengo wa ukulu. 24Ingakale kukala ndi tupili ni chinthu cha mate kupunda kwanu.25Ndande nijiwa sinikalile ndi kuendekela pamoji ndi anyiimwe mwaonche mwachitu kuko ndi kondwelo la chikulupi chanu. 26Ndi ichi sichibwelese chikondwelo chanu ncha chikulu mwa Kristo Yesu, ndande yanga siichulundande yokalapo kwangancho pamoji na mwe. 27Mfunika kukala ukalo wanu mwa maendedwe yofunika mu mau amlungu, chitani chimwecho kuti nikaja nikukuonani pina ngati sini kuonani nivele mwaina chiimile mwa Mzimu umoji ni mpikisanila chikulupi cha mau a Mulungu kwa pamoji.28Msaofyedwa ndi chilichonche chichitidwa na adani wanu, kai nijiwa ndi chilangizi cho wanangika nampho kwanu ni chilangizi cha upulumusi kuchoka kwa Mulungu. 29Anyiimwe mwapachidwa kwa ndande ya Kristo osati ndande yo mkulupalila koma ndi kuvutichidwa mwa iye. 30Pakuti muli ndi mguzano umweuja ngati mdauona kwanga ndi mvela kuti nikali nao mbaka chipano.

Chapter 2

1Ngati kulikutilidwa mtima mkati mwa Kristo. Ngati kulichikondi mkati mwake. Ngati kuli chigwilizano cha Mzimu Oyela. Ngati kulikwelekelela ndi lisungu. 2Chikwanicheni chisangalalo changa pa ganizo limoji mkakala ndi chikondi chimoji, mkala amoji mkati mwa mzimu ndi kukala ndi ganizo limoji.3Msachita mweka ndi dama. Ikapanda kwa kujichicha ndi kwaona wina abwino kupunda kuposa anyaimwe. 4Kila mnaoji wanu wasajipenye iyepe ndi mafuno yake yokha, nampho waone mafuno ya wina kuti ndi ya bwino.5Mkale ndi ganizo ngati walinayo Kikristo Yesu. 6Ingakale iye ngati Mulungu. Nampho siwada jisamale kukhala ngati Mulungu ndi chinthu chakugwilana nacho. 7Pambuyo pake wadajichicha mwene. Wadatenga chifani cha mtumiki. Ndi kuoneka ngati wanthu,wadaoneka munthu. 8Iye wadajichicha ndi kukala ovecha mbaka na kufa, nyita yapamtanda.9Ndipo Mulungu adamkweza kwa mbili. Adampacha jina la likulu kupitilila yonche. 10Wadachitha chimwechi mjina la Yesu kuti bombono lalilonchele likwatame. Mabombono ya alikumwamba ndi alipamwamba pa dothi ndi ali panchi pa dothi. 11Ndi wadachita chimwechi kuthi lilime lalilo nchelo livomele kuthi Yesu Kristo kutti nde Bwana , pa chilemelelo cha Mulungu atate.12Kwaicho, okondedwa wanga ngathi umomdalemekeza siku zonche, osathi ndande ya kukalapo ine nampho nyengo ino wapitilila ingakale ine ndi sakalapo, fumani uombole wanu mwa achinawene kwa mantha ndi kutenthemela. 13Pakuti Mulungu wachitha nchitho mkati mwanu ili wakoze kuganiza ndi kuchitha vinthu vijha vakumkadwilicha iye.14Chitani vinthu vonche popanda kudanda ulidwa ndi mtafu. 15Mchite chimwecho kuthi msadadandaulidwa ndi kukala ndi wana a Mulungu okulupa lila ndi opande kudandaulidwa. 16Gwilani kupunda mau la umoyo ndande ndikale ndi ndande yoelekela siku la Kristo. Ndipo kuthi sindijiwa kuti sindida thamange chajhe sindidavutika chaje.17Ata ngathi ndi pungulidwa ngathi nchembe pamwamba pa golde ndi nchitho yachikulupi chanu, ndikondwa, ndi anyaimwe onche. 18Nampho namwe mkondwe, ndi mkondwe pamoji ndi ine.19Nampho ndikulupilila mkati mwa ambuye Yesu kumuthuma Timotheo kwanu pafupi yapa, kuti ndikoze kuthilidwa mtima yaposindizijwe nkhani zanu. 20Pakuthi ndilije mwina wakapenyedwe ngati kake, waganizo la uzene kwa ndande zanu. 21Wina onche ndidakakoza kwa apeleka kwanu ali ndi vochita vao achinawene pe, ndi osati vinthu va Yesu Kristo.22Nampho mujiwa mate yake, ndande ngati mwana umowatumikila atatawake, nde umo wadatumika pamoji ndiine pakupeleka mau la Mulungu. 23Kwaicho ndi mtuma msanga nyengo yapo sindijiwe chiyani sichindionekele ine. 24Nampho ndikulupilila mkati mwa ambuye kuti ine namwene kuja pafupi yapa.25Nampho ndiganiza kubweza kwanu Epafrodito. Iye ndi mmbale wanga ndi w nchito mnjanga, mtenga ndi mtumiki wanu kwa ndande yanga. 26Pakuti wadali ndi manta ndi wamakumbila kukala nda anyaimwe mwaonche, pakuti mudavel kuti wadali odwala. 27Nde kuti wadaliodwala kupunda pafupi kumwalila, nampho Mulungu wadamlengela lisungu ndi ubwino umeneo siudali pamwamba paifepe, nampho udali pamwamba panga, kuti ndisakala ndi chisoni pamwamba pa chisoni.28Kwa icho ndimbweza msanga kwanu. Kuti yaposimdamuonenche, mkale osangalala pamoji ndi ine sindikale ndachoche dwela mantha. 29Mtanileni Epafrodito mkati mwa mabuye kwa chisangalalo chonche. Alemekezani wanthu ngati iye. 30Kwa ndande ya nchito ya ambuye kuti wadali pafupi kumwalila. wadaluswi cha umoyo wake ndande yakuniombola pa kunithangalila ine pakuti muli pathali ndi ine.

Chapter 3

1Mapeto yake aalewanga msangalale pakati pa ambuye sindione mavuto kukulembe lamincho mau yayaja mkani izi sizikupacheni kuleme kwa bwino. 2Mjipenyelele ndi agalu mjipenyelele ndio chita nchito oyipa jipenye leleni ndi achameneo aya kana maina yao. 3Chifukwa ife ndiachameneo owo taswidi ife ndiachameno ti mpempa Mulungu kwa mpavu za Mzimu Oyela tikulupalila Yesu Kristo ndi achemeneo filibe mpavu ya mofupi.4Atachimwecho ngati kudakakola ndi muutu wokulupalila tupila ine ndikade koza kuchila chimwecho kupunde. 5Chifukwa ndida suwidwa pa nyengo ya nane ni debadwa pa kamule Iziraeli ine wkamu le Benjamini ina ndili Muebrania wa Waebrania pakupeza mfe ndele wa malamulo ya Musa ndi dali farisayo.6Kwa pamvu zanga ndideli chaucho chaucho kanisa kwa muvemelezo uzene wa lamulo. Sini dedandaulidwe pamedandaulo ya lamulo. 7Nampo pakati pamkani izi ndida zione kutizilindi ueneleli twaine ndida welenga ngati zinyalela chifukwa cha kunjiwa Kristo.8Chauzene ndiya walenga yonche yeya kuti yowanangika kuchokela ubwino wakumjiwa Mulungu wanga. 9Ndijilangize mkati mwake andilije lamulola lengalanga kuchokela kuchokela lamulo ikapanda ndilinelolemeo lija lipezeka kwa chikulupalilo pakati pa Kristo ichokela kwa Mulungu lili ndi chiyambi pakati pa chikulu palilo. 10Chapano ndifuna kumjiwa mmenayo ndi mpavu ya uzuka kwake ndi umoji wa mavuto yake. Ndifuna kunganemulidwa ndi Kristo pakati pa moyaluzo ya nyifa yake. 11Mbasako ndikale ndi chikulo pi paku zuka kwa wantu amene adefa.12Osati zene kuti noyapeze ya meneyo kapena kuti ine ndili wabwino kupunda paya meneyo ikapanda ndiji kakamula kuti nikoze kupeza chija chipatikana ndi Kristo. 13Abale wange siniganize kuti nato kuyapeza machitidwe yoya ikapanda ndichiti chimfu chimoji ndiwalila ya mmbuo ndi ya penya ya mchogoro. 14Ndiji kakamula kuti ndifike umo ndifunila dala kuti ndipata mpaso ya ikuhe pa mwamba pakutanidwa ndi Mulungu pakati ndi Yesu.15Taoche ta pulumuko tifunidwa kuganizila chimwecho, ndingati sikale mwino watu waganizile kwa mtundu wosiana pankani iliyonche Mulungu noyenche siwkulangizeni limenelo kwanu. 16Ngati mmenemo ti tiyende ngati umo ili.17Achenjanga ndi chefeni ine apenyechecheni kupunda achemene ayenda ngati umomuyendela amuya imure. 18Ambili alama nde achemeo ntawi zambili no kukambilani ndicho pamo ndikukambileni kwa masozi ambili alamo ngati adawi a mtanda. 19Mapeto yao kuwanengi kudwa chifukwa Mulungu wao tumbo ndi mbwinya zao zilincho nizao aganizile nkani zajiko.20Ikapande maloyatu yaliku mwamba kumeneko tikulupalila mpulumuchi watu Yesu Kristo. 21Siwangane mule metupi yatu yamere yalife mpavu kukale ngati kwa mpavu zimwezija zikozeche kuvimonga vintu voche.

Chapter 4

1Kwa chimwecho okondedwa wanga, anyiyao nikulumbilani, anyiyao ndi chisangalalo nd kolona langa, imenichimiile pakati pa mulungu anyaimwe mabwenji okondedwa. 2Nikupempha iwe Eudia, ndi nikupempha iwe Sintika, mubwezele kugwilizana kwanu kwa mtendele pakati panu, kwa chifuko anyaimwe mwaonche mwawili mudalunjana ndi Mulungu. 3Kwa chazene, nikupemphaninchoni anyaimwe anchito anjanga, atangatileni anyiyawa wachikazi pakuti adatumika pamoji ndi ine pakati popeleka mau la Mulungu.4Pakati pa ambuye masiku yonche. Tena sinikambe, sangalalani. 5Upole wanu ndi ujuwikane kwa wanthu onche, ambuye ali pafupi. 6Msachaucha kwa chinthu chalichonche, pambuyo pake, chitani vinthu vanu vonche kwa njila yopemphela, kupempa ndi kuyamikila ndi chifuno chanu chijiwikane kwa Mulungu. 7Basi mtendele wa ambuye uli waukulu kupitilila kujiwa konche, siupenyelele umoyo ndi maganizo yanu kwa mtandizo wa Kristo Yesu.8Potelapake, achaabale wanga, viganizileni kupunda vinthu vonche vili vauzene, ulemu, haki, ubwino, yali ndi ulemu, pamoji ndi yaja yafunika kuyekeledwa. 9Vichiteni vinthu vonche ivomwajiyaluza, ivomwajilandila ivomwavivela ndi vija mwaviona kwanga ndi io atate watu amtendele sakale namwe.10Nilinacho chisangalalo chachikulu kupunda pakati panu kupitila ambuye pakuti anyaimwe mulangizancho ganizo kwanu pakati pa kujilovya kwanu pakati pa chifuna changa. Kwa chazene, panepo poyamba mudakumbila kunitangatila kwa chifuno changa atangati simudapate malo yonitangatila. 11Sinikamba chimwecho kuti nijipatile chinthu kwa chifuno changa. Pakuti najiyaluza kugwamika katika hali zonche. 12Nijiwa kukala katika hali yachepekela ndi hali yokala ndi vambili. Katika madela yonche ya ine najiyaluza chisisi cha mtundu obwela nyengo yokuta ndi nyengo ya njala yani vambili ndi kukala ofuna. 13Nikoza kuvichita ivi kwa kutangatilishwa ndi iye wanitila mphavu.14Ata chimwecho, mudachita bwino kugwilizana na nane pakati pa masauko yanga. 15Anyaimwe Afilipi mujiwa kuti chiyambo cha mau la Mulungu yapo nidachoka Kumakedonia, palibe kanisa ilo lidanikozecha katika vinthu ivovifunika kuchocha ndi kulandila ingakale anyaimwe mweka. 16Ata yaponidali Kuthesalonike, anyaimwe mudanitumila mtandizo kwa mbili kwa chifuko cho vojifuni vanga. 17Msaganiza kuti nifuna mtandizo, nampho nikamba kuti mpate vipacho vipeleka pindu kwanu.18Nalandika vinthu vonche, ndi chipano najazidwa ndi vinthu vambili. Nalandila vinthu vanu kuchokela kwa Pafrodito. Ndi vabwino vene vonunkila ngati manukato vene kuvomeleka, vonche ndi nchembe iyo imkwadilicha Mulungu. 19Kwa ndande imeneyo, Mulungu wanga siwakuongezeleni chifuno chanu kwa ulemelelo wa ufulu wake katika Kristo Yesu. 20Chipano kwa Mulungu ndi atate wanga ukale ufulu wa muyaya ndi muyaya. Amina.21Moni zimfikile kila muumini katika Kristo Yesu. Okondedwa nilinamwepane akulonjelani. 22Ndi waumini onche pano nikulonjelani hasa anyiwaja wana Akaisari. 23Chipano nema ya ambuye watu Yesu Kristo ikale ndi mizimu yanu.

Colossians

Chapter 1

1Paulo, kapolo wa Kristo Yesupachikondi cha Mulungu, ndi Timotheo m'bale wathu. 2Kwa opemphela ndi abale okulupalila mkati mwa Kristo ali Kukolosai. Neema ikale kwanu ndi mitendele kwa Mulungu atate wathu. 3Tuyamikila Mulungu, tate wa ambuye Yesu Kristo, ndikupemphelani nyengo zonche.4Tavela chikulupi chanu mkati mwa Yesu Kristo, ndi chikondi muli nacho anyiwaja onche asankhidwa kwa ndande ya Mulungu. 5Muli ndichikondi ichi kisa ndande ya chiembekezo cha uzene icho chidaikidwa kumwamba kwa ndande zanu, Muda vela pakati pa chiembekezo icho cha uzene pakati pa mau la uzene la Mulungu. 6Iyo yaja kwanu, mau la Mulungu ili, libala vipacho ndi kuenela pa jhiko lonche. Yakala yochita chimwechi mkati mwanu chivambile paja mudavela ndi kujiyaluza pakati pa neema ya Mulungu mkati mwa uzene.7Ili nde mau la Mulungu ilo mwajiyaluza kuchokela kwa Epafra, okondendwa wanthu kapolo mnyathu, iyeyo nde kapolo wa chikulupi wa Kristo pambuyo pathu. 8Epafra wachita chikondi chanu chijiwike kwaife.9Kwa ndande ya chikondi ichi, chiyambile sikutudavelaizi, tudasiye kukupemphelani. Takala opemphela kuti mkale ndi malango ya chikondi chake cha ulemu woncha wa mumtima. 10Takala opemphela kuti mkoze kwendandi pamvu za ambuye mnjila zokadwa takala opemphela kuti simbale vipacho kwa pochita chabwino nde kuti simkale mkati mwa malango ya Mulungu.11Tupempha kuti mkoze kutilidwa pamvu pa kujikoza kulingana ndi pamvu za ufumu wake pakati pakuvumilia. 12Tukupemphani kuti, kwa chisangalalo simuyamike kwa atate yao akuchetani anyaimwe mkoze kukala osidilwa okulupalila.13Watilamicha kuchokela kulamulo la kumdima ndi kutifikiza pa ufumu wa mwana wake okondedwa. 14Mkati mwa mwanayo twaomboledwa, ndi kukululikilidwa chimo.15Mwana ngati uyo siwaoneka. Ndimbadwa oyamba kwa okonjedwa 16onche.Pakuti kwa iye vinthu vonche vidakonjedwa, ivo vili kumwamba ndi ivo vili pajhiko, vinthu ivo vioneka ndi vosa oneke. Ikakala ndi va nyengo kapena lamulo kapena la mulo kapena alindi pamvu, vinthu vonche vapangidwa ndi iyeyo ndi kwa ndande yake. 17Iyeyo wadalipo pambuyo pa vinthu vonche vagwilina pamoji.18Iyeyo nde munthu wa tupi kuti iyendi nyumba ya mapemphelo, iye ndiyoyamba ndi mbadwa oyambila kuchoka kwa akuta, kwa icho walindimalo yoyamba mkati mwa vinthu vonche. 19Pakuti Mulungu wadakondwa kuti kukwanila kwake kukale mkati mwake, 20ndi kuvanichana vinthu vonche kwa iye kwa njila ya mwana wakeyo. Mulungu wadachita mtendele kwa njila ya mwazi pa mtanda wake. Mulungu wadavanichana vinthu vonche kwa iye mwene, ingakale vinthu va pajhiko kapena vinthu va kumwamba.21Namwecho panyengo imoji mudali alendo kwa Mulungu ndi mdali osavane wake pa njelu ndi vocheta voipa. 22Nampho chipano akugwilizaneni anyaimwe kwa tupi lake kupitila nyifa. Wadachita chimwechi kukubwezani kuti mkale oyela, osadandaulidwe ndi popande kuipa pachogolo pake. 23Ngati simwendekele chikulupi choima ndi kukalacha uzene, Popande kuchochedwa kutali kuchoka pachipenyelelo choima ndi pamphelo ilo mwalivela ili nde mau ilo lida lengezedwa, kwa kila munthu uyo wadapanyidwa kwa kila munthu uyo wadapangidwa pa jhiko. Ili nde mau paine Paulo, ndakala otumika kapolo.24Chipano ndi kontwla mavuto yanga chifuko chanu. Nane nikwaniliza patupi langa chopelewela pa mavuto ya Kikristo, chifuko cha tupi lake, kuti nde nyumba ya Mulungu. 25Ine ndi kapolo wa nyumba mo ya Mulungu, sawasawa ndi nchito ndidapachidwa kuchokela kwa Mulungu chifuko chanu kuika kwa mbili mau la Mulungu. 26Uwu nde uzene obisika uwo udali wa bisika pa viaka vambili kwa vibadwa. Nampho nyengo imo wamasukila kwa onche okulupalila Mulungu. 27Ndi anyiwaja Mulungu wadafuna kuvunukula umo kuli ndi ulemelelo chisili cha uzene mkati mwa jhiko. Ndekuti Kristo wali mkati mwanu nde ulemelelo uwo ukuja.28Utu nde uyo tumlengeza. Tukumuyaluza munthu kwa njelu zonche, ili tumpleke munthu oyela mkati mwa Kristo. 29Pa ndande iyi ine ndilimbikila kuchoka na ndi pamvu yakeyo igwila nchito mkati mwanga.

Chapter 2

1Pakuti nifuna njiwe kuti umo nili ndi tabu ya kulu chifuko chanu, kwa mwaonchhe muli Kulaodikia ni kwa onchhe anyimwe mudapeye nkhope yanga ya tupi. 2Nichita nchito mitima yao ikoze kukulupililidwa kopelekedwa pamoji ndi chikondi ndi ufulu wonche wa vambili vazene vakwamila va njelu ndi kujiwe chisisi cha zene cha ambuye mpulumusi Kristo. 3Kuti nkhani zonchhe za njelu ndi kujiwa zabisidwa.4Nkamba chimwechi kuti munthu waliyonche wasaja kukuitilani voipa kulalika va namiza. 5Pamoji kuti sindili pamoji ndi anyiimwe kitupi, nampho ndili nanyiimwe kimzimu. Nikodwa kupenya ukalo wanu wa bwino ndi nkongono ya chikulupi chanu kw mpulumusi.6Ngati umo mwamladilila mpulumusi ambuye endani ndi iye. 7Mpachidwe machili ndi iye, muuzidwe ndi iye mpachidwe machli kwa chikulupi ngati umo mwayaluzidwa, ndi kumangidwa kwa yamiko la mbili.8Penyani kuti munthu waliyonchhe wasakukodwechani kwa kuchenjela ndi mau yachabe ya unami kutengela ndi malandilidwe ya wanthu kutengela malamulo ya jhiko, asati kulingano ndi mpulumusi. 9Pakuti katika iye msiizilo wonchhe wa Mulungu ukala kalika tupi.10Anyiimwe mwajazidwa ndi uje. Iye ndi mutu wa icho chikozekana ndi malamulo. 11Kwa iye tidaswedwa utonga uo siuchilika ndi wanthu katika kuchochedwa tupi la nyamo, nampho ndi utonga wa mpulumusi. 12Mdazikidwa pamoji ndi iye katika ubatizi ndi kwa njila ya chikulupi katika iye mdahyushidwa kwa nkhongono za Mulungu, uyo wa hyushindwa kuchoka kwa akufa.13Yapo mmdali mwafa kwa kulakwa kwanu ndi kutokuswedwa utonga kwa matupi yanu, adakuchitami amoyo pamoji ndi iye ndi kutulekelela volakwa vatu vonche. 14Adatima kuikumbukilanngawa idalembedwa ndi malamulo yali kumbuyo ndi ife. 15Wadazichoche mkhongono ndi malamulo wadayaita pa danga ndi kuyachita yakale chisangalalo chokoza kwa njila ya mtanda waiye.16Kwa icho munthu waliyonche siwadakulamulani anyiimwe katika kudya ndi katika kumwa, ame kukala siku ya sikukuu ama mwezi wa chapano ame siku za sabata. 17Ivi ni vituncha va ivo vikuja, nampho mtimani mpulumusi.18Munthu waliyoncheyo wasidanyengedwa ufulu wake kokumbila kujichicha ndi kolambila angelo. Munthu wa mtundu umeneo walowa kumkhani yayowayaone ndi kunamizidwa ndi maganizo yake ya kitupi. 19Iye siwaugwililila mutu, ndi kuchoka katika mutu kuti tupi lonche kupitila viwalo vake ndi vifupa kulunjidwa ndi kuikidwa kwa pamoji ndi kukula kwa ukulaji uchochedwa ndi Mulungu.20Ikakala mdafe pamoji ndi mpulumusi kwa vichito va jiko Nampho mlama ngati mchita nchhito pa jiko. 21Msidagwila wala kulakwa wala kugusa. 22Yaya yonchhe yalamulidwa kwa ndande ya kuwananga kukuja ndi kutumikila. 23Malamulo yaya yali ndinjelu za wanthu za konjedwa kwa kujipenya iwe kwa kujichicha kwa mazunjo ya tupi. Nampho zilije ulemelelo pakali pamakumbilidwe.

Chapter 3

1Ikhakhalanjha Mulungu akuuchani pamoji ndi Kristo, vifuneni vinthu va kumwamba uko Kristo wakhala janja la kuchimuna la Mulungu. 2Ganizila kupitila vinthu va kumwamba, osati kupitila vinthu va mjikho. 3Pakuti mwafa, ndi umaya wanu wabisidwa pamoji ndi Kristo kupitila Mulungu. 4Nyengo Kristo yapo swadanechane, iye nda umoya wanu, chipano ndi anyiimwencho simwonekane nayo kupitila ulemelela.5Chipano musie vinthu vilipo kupitila jhiko yaani, chiwelewele, uchafu hamu ya ipa, kuganizila ka ipa, ndi khumbilo, ambavo ndi ibada ya mzimu. 6Ndi kwa chifuko cha vinthu ivi phwai, ya mulungu ikuja pa mwamba pa wana anyiawo selemekeza. 7Ndi kwa chifuko cha vinthu ivi anyiimwe namwe mdaenda nayo yapo mmaishi pakati pao. 8Chipano saina lazima mvichoche vinthu ivi voche yaani mbhumu, kuipidwa, maganizo ya ipa, matukano, ni mau ya chafu yachaka mka mwa mwanu.9Simdanyengana mwachinawene kwa mwachinawene, pakuti mwavala ulemu wa kalendi vichito vaka. 10Mwavala ulemu wa sopano kupitila njeru kuchakana ndi mfano wa yuja wadamuumba. 11Pitila njiru ii, palibe Myunani wa Myahudi, kutainidwa wala kutokutainidwa, asoma sasame kapolo, osati kapela, nampha badala yake Kristo nde vinthu vonche kupitila yonche.12Ngati achagulidwa a Mulungu Oyela akandedwa valani ulemu wa bwina, valani ulemu wa bwina, valani ulemelela wa bwina, ukarimu, kulemekeza, upole ndi kuvumilia. 13Tengelelani anyiimwe kwa anyiimwe. Lengelelanani lisungu kila munthu ndi njake ngati munthu walalamika zidi ya njake, wamlekelele kwa jinsi lija iya ambuye adakulekelelani inyiimwe. 14Zaidi ya vichito vimenevo vanche, mukhale ndi chikondi ambacho nde chimenecha cha chimikizila kupunda.15Mtindele wa Kristo uwachongoze mmitima yanu idalindi kwa ndande ya mtendele iyi ndi kuti mda tilidwa kupitila thupi limoji mkhale ndi kuyamika. 16Mau la Kristo likhale mkati mwanu kwa ulemelela kwa ulemu wanche, yaluzanan ndi kukambana anyiimwe kwa anyiimwe kwa zaburi, ndi nyimbo, kuimba kwa mmitima mwanu kwa Mulungu. 17Ndi chali chonche mchitacho, kupitila mau au kupitila vichito, chitani yonche kupitila jina la Ambuye Yesu mpachoni kuyamika Mulungu atate kupitila iye.18Wachikazi, alemekezeni acha munanu, ngati umo ikwadilichila kupitila ambaye. 19Namwencho wachimuna, akandeni acha kazanu simdakhala wakalipa zidi yaa. 20Wana, alemekezeni akubali wanu kupitila vichinthi vanche, ndande ndande nda umai kwadilichile ambuye 21Anyatate simma yamba wana wanu, ili kuti sadaja kudul nkhumbilo.22Makapolo, alemekezeni achambuye wana kupitila mnthupi kwa vichito vanche asati kwa huduma ya masa ngati wanthu. Okondwelecha pe, ila kwa mtima wa uzene. Muoponi Mulungu. 23Chalichonche mchitacho, chitani kuchaka mmitima mwanu ngati kwa ambuye ndi asato ngati kwa wanthu. 24Mujiwa kuti simlandile mphata ya chindhu kucheka kwa Ambuye ndi Ambuye Kristo uyo mutumikila. 25Ndande waliyonche uyowachita yayo asati haki siwalandile lamula kwa vichintha ivo asati haki yayo wayachita, ndi palibe kupendelea.

Chapter 4

1Anyambuye, chochani amangidwa vindu vili vazene ndi yauzene. Mujiwa mujiwa pakuti mulinao ambuye kumwamba.2Endekelani kukala okulupililika pakati pama pembelo, kalani maso pa ili koyamika. 3Pembani pamoji ndinjila yatu iyi ilikuti Mulungu amasulidwe koma pandande ya mau, kukamba chimsisi cha uzene cha Kristo. Pandande ya ili namangidwa minyororo. 4Ndikupembani kuti mukoza kuliika muzene ngati umo vanibidi kukamba.5Pitani paulemupawaja aokoledwa pabwalo, ndi muokowe ndawi. 6Mau yanu yakala ndimayamiko ndawi zose, ndi yakome mchele pandawi yoje kuti mkoze kujiwa kuti umoyo afunikila mayakgo kila mundu.7Panjito inikuza ine, Tikiko siwachite yofwikana pa iye ndim'bale okondedwa, otumidwa akululupililika, ndiotumidwa mnjatu pakati pa ambuye. 8Ndamtuma kwanu pandande iyi, yakuti mkozi wajiwa vindu vikuzana nafe ndi kuti ukoza kwatila mzimu. 9Ndimtuma pamoji ndi Onesimo, m'bale watu akondedwa okululupilila, ndi mmoji wanu sakukambileni kilachindu chidachitika yapa.10Aristarko, amangidwa mnjatu, wakulonjelani, ndi Marko binamu wake ndi Barnaba mudayalandila kopola kuchoka pake, "ngati siwanje kwanu mlandileni," 11ndi pakuti Yesu waitanidwa Yusto. Uyu yoka ili watailidwe ndi yao agwila njito anjatu panjila ya ufumu waMulungu. Akala ndilaha kwanga.12Epafra wakulonjelani iye nimmofi wanu ndi atumidwa wa Kristo Yesu. Iye wachita kujituma pakupembela panjila, yakuti mkoze kuima pauzene ndi kujiwichidwa pauzene pachikondi cha Mulungu. 13Pakuti muyamikila, kutiwangwila njito kofituma panjila yatu, payao aomboledwa Laodikia payao alipo Hierapoli. 14Luka, yufa mfumu okondedwa, ndi Dema akulonjelani.15Mwalonjele abale watu alipo Laodekia, ndi nimfa, ndikanisa lija lilipo mnyumba mwake. 16Utenga u yaposakale wasomedwa mutima mwanu, isomedwe paja pajapakanisa la wa Laodikila, namwe muya aminishe muya some ija baluwa kuchoka Laodikia. 17Kamba pa Arkipo, "penyani ija njito iyo wailandila pakati pa ambuye, kuti itumika kuichita."18Moni iyi ije pajanja panga namwene Paulo uyikumbukile minyololo yanga ufumu ukale ndi anyiimwe.

1 Thessalonians

Chapter 1

1Paulo, Silwano ndi Timotheo kwa kanisa la Wathesalonike mwa Mulungu atate ndi AmbuyeYesu Kristo. Mwawi ndi mtendele ukele namwe.2Tichicha mayamiko kw Mulungu nyengo zonche kwa chifukochanu mwawonche, nyengo tikuchulani pa mapembhelo yatu. 3Tiikumbukila popande kuimikila pachogoo pa Mulungu ndi atate watu njhito yanu ya chikulupi kulimbicha chikondi, ndi chidekilo uwo opilila kwa chifuko cha pambuyo pa Ambuye Yesu Kristo.4Abale yawomkondedwa ndi Mulungu tijhiwa kutanidwa kwanu. 5Ndi umo utenga watu umonda jhela kwa anyiimwe osati kwa maupe, akapandancho kwa mphamvu mwa mMzimu Oyela, ndi kukulupalila kwa mtundu umwewo, mjiwancho ire tidali wandhu amtundu wanjhi mmojhi mwanyiimwe kwa ndande yanu.6Mdali wandhu wakuliyesa ife ndi Ambuye, ngatiumomdalandila mau pa mavuto ndi chimwemwe chichoka kwa Mzimu Oyela. 7Ndi yochekala yake mdali chifanizo cha wonche pa Makedonia ndi Akaiya yawo akulupalila.8Pakuti kuchokela kwanu mau la Mulungu layenela konche ndi osati kwa Makedonia ndi Akaiya yokape, Pambuyo pake, kwa kila pamalo chikuhepi chanu pa Mulungu yayonela konche. Ndi yochokela yake, sitifuna kunena chalichonche. 9Pakuti anyiiwo achinawene aweze kubwela kwatu kudali kwa mtundu uti pakati panu. Achezelela umo mdamng'ana mukila Mulungu kuchokepa chosepa ndi kumtumikila Mulungu wali wa umoyo ndi wazene. 10Adachocha nkhani kuti mulindilila mwana wake kuchokela kumwamba, uyo wa yhuka kuchokela kwa akufa. Ndi uyu ndi Yesu; uyowatiika mtendele kuchokela mumphweyi ikujha.

Chapter 2

1Abale, mwachinawene mujiwa kuti ulendo watu kwanu adali osati chaje. 2Mjiwa mmayambo tidavutika ndi adatichiticha nchoni, kuja Kufilipi, tikali osaje kwanu Kuthesalonike, ingakale kudali mkangano wa mbili, Mlungu watu wadalipacha mphavu ya kukulalikilani utenga wake wabwino.3Chinthu icho tichisa kwanu osati la lilindila unami kapena mtima oipa, sitifuna kumnyenga walienche. 4Ife tinena nthawi zonhe ngati umo wafunila Mulungu chifukwa wadationa tili ndimate, wadatipacha utenga wa bwino, osati kufuna kwatu kuokondwecha wanthu nampho Mulungu, iye wajiwa mitima yatu mbaka.5Ngati umo njiwila ife sitidakambe msu yopembeza kapena mau yo bisa, Mulungu ndin mboni. 6Sitidafune uelekelo kuchoka kwa wanthu kapena kwanu kapena kuchoka kwa munthu waliyonche7Ingakale ife otumidwa a Kristo, tidakafu vinthu vakuti kuchoka kwanu, nampho ife tidali ojichicha pakati panu, ngati umo ali amai kwa wana wao. 8Tidakukondani kupunda, tidafuna kuti tigwilizane osati pa nkhani ya utenga wa bwino, nampho ndimoyo watu tawefe ndande mwakala okondedwa watu. 9Abale mkumbkila nchito ndi mavuto yatu, usikundi usana, tidachitanchito, kuti tisada mlemelela munthu walionche nyengo ndi kulalikilani utenga wa Mulungu.10Anyiimwe ndi mboni, Mlungu nae mboni, ntundu umo tidakalila kwanu mkulupalila, kwa kuyera ndi malinga popande. 11Njiwa kuti ife tidamchitila kila mmoji wanu ngati muja atate umo achitila wana wake tidakuchiani ndi kukuninkhani mtima. 12Kuti mkale moyo omkondwelecha Mlungu iye wakutanani mlowe mu ufumu ndi kuyera kwake.13Kwa ndande imeneyo, timuyamika mlungu nthawi zonche, pakuti yapo mdalandila kuchokela kwatu utenga wa Mlungu mdalandila osati ngati mau langu munthu nampho mdalandila ngati mau la zene la Mlungu limene lichita nchito mkati mwanu.14Kwa icho abale mkale wanthu oyesa makanisa ya Mlungu yali mwa Ayuda mwa Kristo Yesu. Pakuti anyiimwe mdavutika mu vinthu vija kuchokela kwa Ayuda. 15Adali Ayuda nde yao adaaa Ambuye Yesu pamoji ndi olosa, Ayuda nde adatitopola tichoke kubwalo, samkondwelecha Mlungu ndi adani a wanthu onche. 16Adatikaniza tisakamba ndi wanthu amaiko ina angapeze kupulumchidwa, zochatila ndi kuti aendekela ndi machimo yao, potela mphwai siibwele kwao.17Abale, kulekana kwatu na anyiimwe kudali kwa nthawi ya ifupi, ndi kudali kwa tupi osati kwa mzimu, pambuyo tidapata kumbilo la kukuonani. 18Pakuti tidafuna kuja kwanu, ine Paulo, mara kamoji ndi kujancho nampho satana wadatichekeleza. 19Pakuti kupilila kwatu ni chiyani pambuyo kapena chimwemwe, kapena chisoti cha ulemu, chojidamila pamaso pa Ambuye Yesu nyengo yobwela kwake? Bwa osati anyiimu mwapunda ngati umo ali wina. 20Pakuti anyiimwe kuyera ndi chimwemwe chatu.

Chapter 3

1Yapo tidali sitikoza kudikila kopitilila, tidaganizila kuti idali bwino kukalilila ku Athene kuja ife teka. 2Tidamtuma Timotheo, m'bale watu ni otumika wa Mulungu katika mau la mpulumusi, kwakamilishani kwa tondoza kulingana ni chikulupi chanu. 3Tidachita yaya dala kuti wasakalapo waliyonche wa kuchika kuchokana ni azunjo yaya, pakuti anyiimwe mjiw kuti tatosankhidwa kwa chifuko cha ili.4Cha zene, muda tidali pamoji ni anyiimwe tidachogolela kukambilani kuti tidali pafupi kupata mazunjo ni yameneyo yadachokela ngati umo mjiwila. 5Kwa ndande ii, yapo nidali simkoza kudikilancho, nidatuma dala kuti nipate kijiwa juu ya chikulupi chanu. Pina muyese wadali pina wayesa, ni nchito yatu yakala yachaje.6Nampho Timotheo wadaja kwatu kuchokela kwanu ni walipelekela nkhani ya bwino juu ya chikulupi ni chikondi chanu. Wadatikambila kutimuli ni kukumbukila kwa bwino juu yatu, ni kuti mkumbila kutuona ngati umonaye tikumbila kukuonani anyiimwe. 7Kwa ndande ii abale tisanalala kupunda ni anyiimwe kwa ndande ya chikulupi chanu, kaika mavuto ni mazunjo yatu yonche.8Ka chapano tikala, ngati mkaina bwino kwa Ambuye. 9Chifuko ni mayamiko yati timpache Mlungu kwa ndande yanu, kwa chisangalalo chonche tilinacho pachogolo pa Mlungu juu yanu? 10Tipempha kupunda usiku ni usane dala tikoze kuziona nkhope zanu ni kuongezelani chichepekela katika chikulupi chanu.11Mlungu watu ni Atate wene, ni Ambuye watu Mpulumusi atuchogoze njila yatutifike kwanu. 12Ni Ambuye akuiteni muongezeke ni kupitilila katika chikondi, mkakondana ni kwakonda wanthu onche, ngati umo tikuchitilani anyiimwe. 13Ni wachite chimwechi dala kuikwimicha mitima yanu ikale bila kulaumidwa katika kuyela pachogolo pa Mlungu watu ni Atate watu katika kufika kwa ambuye Mpulumusi pamoji ni Oyela wake onche.

Chapter 4

1Ndiposo abale tikutilani moyo ndikukusiini kwa Yesu Krisyto ngati umo mudalandilile utenga kuchoka kwatu ivo ifunikila kupita ndikukwadilicha Mulungu panjila iyi ndiposo mupite ndikuchita kupunda. 2Pakuti mujiwa ndi manyanji yayo tidakuningani kupitila Ambuye Yesu.3Pakuti yaya ndechifuno cha Mulungu, kuelesedwa wanu kuti muepuke chingololo, 4pakuti kila mmoji wanu wajiwa njila yomiliki mkaziwake mwene pakati pa ufulu ndi ulemu. 5Usidakala ndi mkazi pandane yachifuno chatupi (ngati amjiko yao samujiwa Mulungu) 6Wasadakalapo mundu walionje uyosiwa yomboke malile ndi kumlakwila mbale wake pandande yajamboili. Pakuti mulunde mwene walipa chisasi pavindu vonje vii ngati umo tuchongolelela kukukambvani ndikuona.7Pakuti Mulungu sadatuta kwa uchafu, ndipo koelesedwa. 8Chocho uyowalikana ili tuwakana wandu ndipo wamkana Mulungu uyo waniha mtima oyela wake.9Kupitila chikondi wabale, palibe aja yamundu walionje kukulembela pakuti mayaluzidwa ndi Mulungu kukondana anyiimwe kwa anyiimwe. 10Ndiposo, mudachita ivi vonje kwa abale ali Makedoniya yonje, nambo tikusihini, abale, mchite hata kuposa. 11Tikusihini niukumbile kulama maisja yodeka, kujiwa njitozanu ndikuchita njito kwamanja yanu, ngati umo takulamulilani. 12Chitani yaya ili ukoze kulingana bwino ndi kwaulemu kwayao alikubwal ndi njito kwamanya ndapunguzika ndi chofua chilichonje.13Sitifuna anyiimwe muvane navo vamtila, anyiimwe abale, pamwamba yao angona ili msidaja kudabwa ngati wina alibe chikulupililo kuusu ndawi ikuja. 14Ingakale tivananavo kuti Yesu wadafandi kukajo, chocho Mulngu siwakupelekeleni yamoji ndi Yesu yao angona kunyifa pakati paiye. 15Pandande yayameneyo tikukambilani anyiimwe pamau la Ambuye kuti ife tilimoyo yao sitikalepo pandawi yojiwa kwa Ambuye, uzene sitachongolela waja, yao angona kunyifa.16Pakuti Atate wene sachike kuchoka kumwamba siwaje nimau yayakulu, pamoji ndi mau ya angelo wa mkulu, pamoji ndi palapanda ya Mulungu, nao afa pakati pa Kristo sazuchidwe huti. 17Ndiposo ifetili hai, tasala, sitichongozane kmitambo pamoji nao kumulaki Ambuye mu hewa. Panjilaiyi sitikale nda atate ndawi zose. 18Pachocho. mufalijiane anyiimwe kwa anyiimwe ka mau yaya.

Chapter 5

1Chipano, kwa nkhani ya nthawi ya nyengo, abale, palibe haja kuti hinthu chalichonche chilembedwe kwanu. 2Pakuti anyiimwe mwachinawene mjiwa kwa uzene kuti siku ya Ambuye ibwela ngati mnkhungu yapo wakuja usiku. 3Paja akamba kuli "mtendele," ndeyapo kuwananga kukujelani ghafla, ndi ngati uchungu umaujela mama mwene mimba. Siakwepa kwa njila yaliyonche.4Nampho anyaimwe, achabale palibepo ku mdima hata ija siku ikujeleni ngati mnkhungu. 5Pakati anyaimwe mwaonche di wana adangalila ndi wana ausana, ife osati wana ausiku au akumdima. 6Mchemwecho basi, situdagona ngati winancho umeagonela ila tikeshe ndi kukala machenjela. 7Pakuti anyiyawo agona agena usiku ndi anyiyawa alnjela usiku.8Pakuti ife ndi wana aisana, tukale machenjera tavale ngao ya chikulupi ndi chikondi, ndi chisati cha chuma, ambayo ndi uzene wakualamichidwa kwa nyengo ikuja. 9Pakuti Mulungu siwadatusakhule mmayambo kwa chifukwa cha kuipidwa, ila kwa kupata kulamichidwa kwa njila ya Ambuye Yesu Kristo. 10Iye nde wadatufela ili kuti, takhale masa au tagona, sitiishi pamoji aye. 11Chipano, mthandalone ndi kujengana anyaimwe kwa anyaimwe, ngati umo muli tayari muchita.12Abale, tikupemphani mwajiwa anyiwaja anyiyawo atumiki mkati mwanu ndi anyiwja ali pa mwamba panu kupitila Ambuye ndi anyiwaja anyiyawo washauri. 13Tikupemphanchani mwajiwe ndi kwaaninkha ulemu kupitila chikondi kwa chifukwa cha nchito yao, mnkhale ndi mtendele mkati manu anyaimwe mwachinwene. 14Tukupemphani, achabale; mwaonye anyiyawo siaenda kwa utaratibu, athileni mtima anyiyawa adulakhumbilo, atangatilani ali anyonge, ndi mkhale ndi kuvumilia kwa onche.15Penyani wasidakhalapo munthju waliyonche uyowalipa choipa kwa choipa kwa munthu waliyonche. Badala yake, chitani yali ya bwino kwa kila mmoji wanu ndi kwa wanhu onche. 16Furahini siku zonche. 17Pemphani bila kulema. 18Muyamikileni Mulungu kwa kila chchito, kwa chifukwa chimenecho nda chikondi cha Mulungu kwanu kupitila Yesu Kristo.19Msidathimiza mziu. 20Msidakupepula kurosa. 21Viyeseni vichita vonche. Mligwile ilo lili bwino. 22Jichocheni kila kuoneka kwa voipa.23Mulungu wa mtende wakukamilicheni kupitila kuyela, mzimu, mtima ndi nthupi vitamandidwe bila makosa kupitila kuja kwakwe Ambuye wathu Yesu Kristo. 24Iyo wkutanani ndi okulpalika, naye nde uyowachita.25Achabale, tupemphelaninchoni. 26Alonjeneni achaabale onche kwa busu lo ela. 27Ndikupemphani kupitila Ambuye kuti karata ii isomedwe kwa achaabale onche. 28Mwawi wa Ambuye wathu Yesu Kristo ikhale pamojhi namwe.

2 Thessalonians

Chapter 1

1Paulo, Silwano ndi Timotheo mwawantu athesalonike mkati mwamulungu tate watu ndi olemekezake Yesu Kristo. 2Mwawi ukale namwe ndi mtendele uchoke kwa atatewatu ndiko olemekezeko a Yesu Kristo.3Yofunika ife kumuyamika Mulungu ntawi zonche chifukwa chanu achabale mate ndimo tifuni dwila chifukwa chikulupi cheme kukula kupunde ndichi kondamo chanu kwa waliyonche chiende kele. 4Mmwemo tea chinewefe tiko mbilane kwa ulemu wa pamwamba pakatipanu pa katikati pa makanisa ya Mulungu.Tukambilane nkani ya kuleka lelana kwanu ndi chi kulupi mulinacho pa mevuto yoche tukambilane pankani ya movuto yafunika. 5Ichi ndichi zindikilo chole mulo la bwino la Mulungu meyanko yake ndikuti anyiimwe muwelengedwe kuti mwaloledwa kulowa kuu ufulu wa kumwamba umeneo kwa chifukwa chake mwavutika.6Chifukwa niuzewe kwa Mulungu kwapacha mavuto acho maneo akupachoni mavuto anyiimwe. 7Ndikukupachoni mtendele anya imwe mwapachidwa mavuto pamoji ndiife. Siachite chimwechi ntawi ya kulangizidwa kwake olemekazeka watu Yesu Kristo kuchokela kumwamba chimoji moji ndi angelo wa mpavu zake. 8Pakati pa mogezi ya moto siali pidwe ya maneyo ada ya chita acho meneo siamjiwa Mulungu ndi ado meneo siali vemela mau la Mlungu.9Savutike ndekupwete kedwelatu ntawi yonche ndi kuikidwa pampepete pameso pa Mulungundi ulemelelowapamvu zake. 10Siachite pantawi jobwelo dele kuti kulemekezedwa ndi wantu wao ndi kudabwa ndiache alolele, chiukwa kuvemelezeka kwatu kwami.11Chifukwa paichi tu kupembelani anayaimwe ntawi zonche tukupembelani kuti mulungu watu wakuwelenyeni kuti mda vemeledwa kutamidwa. 12Timpepmpa nkaa ize ala lekuti mpeze kuliika pamwamba ino la ambuye watu Yesu Kristo Tipempa kuti mpeze kuikidwa ndiye chifukwa veneleliwake Mulungu ndi olemekazake Yesu Kristo.

Chapter 2

1Chapano kuhusu kubwela kwa ambaye watu Yesu Kristo ndi kutikusanya pamoji ili tikale nae: tikupemphani anyaimwe achaabale watu. 2Msachauchidwa ndi kuvutidwa kwa lahisi kwa mzimu, kapena kwa utena kapena kwa kalata iyo ionekana kuti yachoka kwatu, ikakamba ya kuti siku laambuye tayali lafika.3Munthu wasakunyengani kwa walivonchevo. Pakuti sifika mbaka lija mau lichokele poyamba ndimunthu alakwa wamasulidwe, yuja mwana olakwa. 4Uyu ndiye ochucha ndi kujikweza mwene wakamchucha Mulungu ndi chalichonche chipempeledwa. Ndi chifuko chake chikala mnyumba ya Mulungu ndi kujilangiza kuti iye ngati Mulungu.5Bwanji, sumukumbukila kuti yapo nidalinamwe nidakukambilani pakati vinthu ivi? 6Chipano mujuua chija chimchekeleza ili kuti wakoze kuvunukulidwa kwa nyengo yokwana yaposifike. 7Pakuti chisisi cha yuja munthu dakwa ichita nchito mbakana saino, ila tu kuli uyowamchekeleza saino mbakana yapo simachochechedwe panjila.8Nde yuja mwene kulakwa yaposimavunukulidwe, ndipo iyeyo ambuye Yesu sampe kwa mphumu ya pakamwa pake, ambuye samchite kuti osati chalichonche kwa ufunuo wa kubwela kwake. 9Kubwela kwake kwa yuja mwenekulakwa siukale kwa ndande ya nchito ya satana kwa mphavu zonche, chizindikilo ni vintu vozizwicha va unami, 10ndi unami onche aipa vintu ivi sivikalepo kwa anyiwaja asokelela, ndande yake sada chilandile chikondi cha zene chifuko chakuomboledwa kwao.11Kwa ndande imeneyo Mulungu wakutumila ni nchito iliyoipa kuti muamini unami. 12Mayanko yake ndikuti onche salamulidwe, anyiyao sadaamini uzene popande anyaiwo kujisangalalicha.13Lakini tifunika timuyamikile Mulungu kila nyengo kwandande yanu achaabale mukondedwa ndi ambue. Chifuko ambue ada kusangulani anyaimwe ngati malimbuko ya kuomboledwa ndi kutakasika Mzimu ndi mtendele pakati pa uzene. 14Ichi ndeicho adakutanilani anyaimwe, kuti kupitila mau la Mulungu mukoza kupata ufulu wa ambuye watu Yesu Kristo. 15Kwa chimwecho, abale imani imala. Mvane nao utamaduni uo mwayaluzidwa, kwa mau kapena kwa kalata.16Chipano ambuye watu Yesu Kristo mwenendi Mulungu tate watuadatikonda ndi kutipacha chisangalalo cha muyaya ndi kujutuma kwa bwino kwa chifuko cha ukalo ukuja kupitila nema. 17Watondoza ndi kwachita chiimile mitima yangu katika kila mau ni nchito ya bwino.

Chapter 3

1Nichipano, abale, tipempheleni Maula Ambuye likoze kuenela ndikulemekezedwa, ngati umo idali kwanu. 2Pemphani kuti tikoze kuokoledwa kuchoka kula kwana ndi wantu olakwa, pakuti osati onche anyio aamini. 3Nampho ambuye okulupalika, yao sakulimbicheni imwe ndi kukulindanikuchokela kwa yuja mdani.4Tili ndimphavu kwa ambuye kwaajili yanu mchita ndi simuendekele kuchita vintu ivondidawatuma. 5Ambuye akoza kutichogoza mitima yanu ndi chikondi ndikuvumilia kwa Kristo.6Chapano nikutumani, abale, pajina la ambuye Yesu Kristo, kuti uyepuke ndikila mbale uyo walama ndi maisha ya ulesi ndikuchokana ndi mila izo mdalandila kwatu. 7Pakuti anyiimwe mwachinawene muyajiwa ndisawa kwanu kutiesa ife, sitidakale kwa niamba mwanu ngati anyii waja adali alibe ulemu. 8Ndisinidaje chakuja chamuntu walienehe kuchilipila, pambuyo pake, tidachita nchito usiku ndi masana kwa uchito zolimba ndi kwa mavuto, kuti sitidakakoza kukala ndi katundu kwa walienche ndi anyiimwe. 9Tidachita chimweecho pakuti tidalibe malamulo pambuyo pake, tidachita chimwecho ili tikale mano kwatu, ili kuti mkakutiesa ie.10Ntawi yapotidali pamoji namwe tidakutumani, mkakala mmoji wanu siwauna kuchita nchito opande kujipenyelela. 11Pakuti tivela apita kwa ulesi, mmalo mwanu. Sachita nchito nampho pakuti pake ndi wantu opande kujipenyelela. 12Chapano ameneo tituma ndikukuofyani kwa ambuye Yesu Kristo, kuti mchite chintu koji penyelela ndikudya chakudya chao wene.13Pakuti ife, abale, msidaa mtima kupita kuchita yayo yaliyobwino. 14Wakaka munthu walionche siwafuna kulemekeza mau latu kupitila walaka uno mukale masandi si mdavananae pamoji naye ili kuti waone manyazi. 15Msidatengera ngati,mdani, nampho mumlangize ngati m-bale.16Ambunye anntendelewene wake aapache mtendele ntawi yalionche ndi nyengo zonche.Ambuye akale namwe maonche. 17Li nde moni yanga, PAulo, kwa janja langa namwene ndi chidindo pakati pawaka, umo ndili nilembavo. 18Mwai wa ambuye watu a Yesu Kristo ikoze kukala namwe maonche.

1 Timothy

Chapter 1

1Paulo atumika wa Mpulumusi kuchatana ndi lamulo la Mlungu ndi olamicha watu Mpulumusi wali ndi kujilingila kwatu. 2Kwa Timotheo mwana wanga wa zene kwa chikulupalilo. Mwawi kulekelela ndi mtendele zichoka kwaMulungu atate ndi Mpulumusi Ambuye watu.3Ngati umo nakupemphelani yaponachoka kupita Kumakedonia, ukale kueyeso dala kuti ukoze kwalamula wanthu akuti asayaluza mayaluzo yanjake. 4Ndi asavechela nthano ndi welengedwe za kamu zilijendi potela. Yaya yasababishidwa ndi kubishana kwa mbili osati kwatangatila kuendekela mtete w Mlungu wa chikulupi.5Nampho potela pa lamulo ili ndi chikondi chichoke pa mtima wa bwino pa ganizo la bwino ndi pachikulupi cha Zene. 6Wanthu akumoji lakosa limenelo adayaleka mayaluzo yaya ndi kung'anamukila mau yopande mate. 7Ayuna kukala olalikila olamula, nampho siajiwa ichoakamba au ichoalimbikiza. 8Nampho tijiwa kuti lamulo ndi labwino ngati munthu walitumikile kwa zene.9Tujiwa kuti, lamulo lidatungidwe kwa chifuko cha owananga lamulo ndi olakwa wanthu siali abwino ndi anyiyao achimo, ndi anyiyao alije Mlungu ndi olakwa. Yaikidwa kwa chifuko cha akupa atatawao ndi anyazimai wao kwa chifuko ya akupa. 10Kwa chifuko cha amalaya, kwa chifuko cha wanthu achigololo, kwa chifuko anyiwaja agwila wanthu ndi kwachita mambowa, kwa chifuko cha aunami, ndi waliyonche wali asagwilizane ndi mayaluzo ya chikulupi. 11Mayaluzo yaya yachokana ndi mau ya ubwino waMlungu wali kudalisidwa kuti ndiiye nachulupalilidwa.12Nimuyamika Mpulumusi Ambuye watu. Wadanipache mphavu, pakuti wadaniwelenge ine kuti okulupalilika, ndi wandamika katika kutumika. 13Nidali munthu otukana wakwaipicha ndi munthu wa ndeo. Nampho nidapata kulekeleledwa kwa ndonde nidachita kwa kuwewela kwa kutokulupalila. 14Nampho mwawi wa Mulungu watu wajala chikulupi ndi chikondi chili katika Mpulumusi.15Mau ili ndi lokulupalilika ndi lifunika kulandilidwa ndi onche yakuti Mpulumusi wadaja pajiko kulamicha ali ndi chimo. Ine ndi oipa kwapita onche. 16Nampho kwa ndande ii ine napachidwa kulekeleledwa dala kuti mkati mwanga ine oyamba kwa vonche Mpulumusi walangize kuembekeze konche wadachita chimwecho ngati chilangizo kw onche amkulupalile ije kwa chifukwa cha umoyo wa muyaya. 17Ndi saino kwa Mfumu walije potela, siwakufa, siwaonekane Mulungu yaka, ikale ulemu ndi ufulu muyaya ndi muyaya. Zene.18Niliika langizo ili pachogolo pako Timotheo, mwana wanga. Nichita chimwechi kuchatana ndi ulose wachochedwa yapo poyamba kukulanga iwe, dala kuti ufunike katihendeo ya bwino. 19Chita chimwecho dala kuti ukale ndi chikulupi ndi ganizo la bwino. Wanthu wina ayakana yaya adaya chikulupi. 20Ngati yuja Himeneyo ndi Alekizanda anyiyao nampacha satana dala ayaluzidwe asamtukana Mulungu.

Chapter 2

1Kwaicho payamba ndikupemphani kuti pakhale mapembphelo, ajowapemphera wanthu wonche. 2Ndande ya mafumu ndi wantu wonche alimmaudindo kuti likhoze kukhale umoyo wa bata ndi mtendere tijitamande Mulungu ndi ulemu. 3Ichi ndi chabwino ndi chovomeleka pamaso pa Mulungu Mpulumusi wanthu. 4Iye wakhumbila kuti wanthu wonche aomboledwe ndiakhoze kujhiwa uzene.5Pakuti pali Mulungu mmojhi, ndi kuli mkala pakati mmojhi pa Mulungu ndi wanthu iyeyo nde Kristo Yesu. 6Iye wadajichocha mwene kuti wakhale muomboli wa wanthu wonche, ngati umboni pa nthawi yake. 7Nchifukwa ichi, ine namwene wake adandichita kukhala mtenga wa mau la Mulungu ndi mtumiki. Ndikhama zene sindikamba unami. Ine ndi mphuzisi wa wanthu amitundu ina mau ya chikulupililo nde zene.8Kwaicho kila pamalo ndifuna wachimuna ajiphempha ndikukweza manja yoyera popande nkwiyo kapena mantha. 9Chomwecho ndifuna wachikazi ajivala vivalo ivo vavomeleka, wanjelu ndi ulemu asakhala ndi tsitsi lomangidwa kapena golide, mkanda wa mtengo wa patali. 10Ndifuna ajivala vivalo aenela kuvala wachikai avomela kukhondwecha kujela vichito vabwino.11Wamkazi wajiyaluze kukhala chete ndi ulemu wonche. 12Sindilola kuti wamkazi wajiyaluza, kapena kukhala olamulila wachimuna, ikapanda wajikala chete.13Pakuti Adamu wadali oyambila kulngedwa, pambuyo pake Eva. 14Adamu siwadanamizidwe, nampho wamkazi wadanyengedwa ndi kupenya lamulo la Mulungu. 15Ingakale siwaomboledwe kujela kubala wana ndi ndi kuyera mtima ndi njelu za bwino.

Chapter 3

1Mkambo uu ni okulkupalilika; ngati munthu wakumbila kukala, wakumbila nchito yabwina. 2Kwa icho oimilila ni lazima wasakala ni lawama. Nilazima wakalewammuna wa wamkazi mmoji. Ni lazima wakale ni kiasi, busara, wali ni utaratibu, okaribisha wanthu. Nilaima wakale ni uwezo wa kuyaluza. 3Wasakala otumikila mowa, wasakala wa ndeo ila mpole wali ni mtendele. Ni lazima wasakala uyo okonda ndalama.4Ifunika kwaimilila bwino wanthu akukomo lake mwene, ni wana wake ifunika kumlemekeza kwa ulemu onche. 5Chifuko ikakala munthu siwajwa kwaimilila wanthu akukomo lake mwene, mene, walilele bwanji kanisa la Mlungu?6Wasakala okulupalila wa chapano, dala kuti wafika ajivuna ni kugwa katika lamulo ngati yuja olakwa. 7Lazima pia wakale ni sifa ya bwino kwa onche ali kubwalo, dala wasaja kugwa kwa nchoni ni mchelo wa oipa.8Mashemasi, chimwecho afunika kukala anyiyao ufunika ulemu, osakala ali ni tabia ziwili, asalewa kopitilila au kukala ni kukumbila. 9Akoze kuipenyelele kwa mtima wa bwino ija zene ya chikulupi yaikidwa padanga. 10Akale pia avomelezedwa poyamba, dala akoze kutumikila kwa ndande aliye kulaumidwa.11Wachikazi chimwecho akale ali ni ulemu, asakala osanamizila. Akale ni pang'ono ni okulupalilika kwa mambo yoyote. 12Mashemasi ni lazima akale wachimuna awamkazi mmoji mmoji. Lazima akoze kwaimilila bwino achana wao ni apakomo lake. 13Pakuti anyiyao atumikila bwino apata kuina bwino ni kujikulupalila papakulu katika chikulupi chili katika mpulumusi.14Niyalembamambo yaya kwa iwe, ni nikulupalila kuja kwako chimwechi pafupi. 15Nampho ikakala nichedwe, nilemba dala upate kujiwa namna yopita katika nyumba ya Mlungu, ambayo ni kanisa la Mlungu wali wamoyo, chokwelela ni chitandizo cha zene.16Nisiipingika kuti zene ya Uungu waikidwa wazi ni waukulu, "wadaonekana katika tupi, ni kumlangiza katika mzimu, wadalangizidwa ni angelo, wadatangazidwa pamoji ni Maiko, wadakulupalilidwa ni jiko ni wadatengedwa kumwamba katika ufulu."

Chapter 4

1Chipana mzimu ukamba kuti nyengo zikuja baadhi ya wanthu siasie chikulupi ndi kukala makini kuvechela mizim yamtila ndi mayaruzo ya mizimu yayo siyayaluzidwe pakati pa mtila ndi unafiki. 2Maganizo yao siyabadilishidwe.3Siwawakanize kukwata ndikulandila vakudya ambava Mulungu wadavilengedwa vitumike kwa kuyamikila mkati mwaa akulupalila ndi anyiyawo ajiwa uzene. 4Kwa chifukwa kila chitu ambacho Mulungu wakukambila ndi chabwino, palibe ambacha tuladila kwa kuyamikila chifunikana kukanidwa. 5Kwa chifukwa chichukidwa kupitila mau la Mulungu ndi kwa njila ya mapemphelo.6Ngati siuyiike vichito ivi pachogolo pa achabale, siukale mtumiki wa bwina ambayo wayachata. 7Nampho liale adisi za pajiko ambazo zianedwa ndi wachikazi midala. Badala yake yake, jyaluze umwene pakati pa kumjiwa mulungu. 8Pakati mazoezi ya nthupi yafa; pang'ana, nampho kumjiwa Mulungu kufa sana kwa vichito vonche watuza ahadi kwa umoyo wa saino ndiuja ukuja.9Uumbe uu ndi wakukulupalidwa ndi ufumnikana kuvomelezedwa kabisa. 10Pakuti kwa chifukwa ichi tuangaika ndi kuchita nchito kwa bidii sana, pakuti tulindi ujasiri mkati mwa Mlungu wali waoyo, ambaye ndi olamicha wanthu onche, nampho hasa kwa anyiwaja akulpalila.11Uyakambne ndi kuyaluza vichita ivi. 12Munthu waliyenche siudaudelela unyamata wako. Pambuyo pake, ukale chifanizi kwa onche akulupalila pakati pakamba, kuyenda chikandi, kulupalika, ndi usafi. 13Mpaka yaposindije, limba pakati pa kusama, pakati pa kuanya, ndi pakati pa kuyaruza.14Usidaisia chipawa chili mkati mwako, ambacho udanikidwa pitira orosa, kwakuikidwa manja ndi midala. 15Ujali vinthu ivi uishi mkati mwa yameneyo ili kukula kwako kukale wali kwa wanthu onche. Penyelela sana kuenda kwako ndi mayaruzidwe. 16Limba pakati pa vichito ivi. Pakuti kuchita mchimwecho siujitamiche umwenendi anyiwaja akuvela.

Chapter 5

1Usidamkalipila wamuna wazeeka ndi poso unikhe mtima ngati atate wako wanikhe mtima anyamata wachimuna ngati achabale wako. 2Watile umoyo wachikazi azee ngati mama zao, ndi achikazi anyamata ngati dada zake pausafi onje.3Alemekezeni ajane, waja ali ajane zene zene. 4Nambo ngati mjane walibe mwana pena ijukulu, asieni huti ajiyaluze kulangiza ulemu kwawandu anyumba yao achinawne aieni walipiche azazi wao vabwino, pakuti iyi kwadilicha pachongolo pamnungu.5Nambo mjane wazene zene yuja wasiidwa yoka nayo waika chikulupi chikulupililo chake kwa Mulungu nyengo zoje walama ndi kusali ndi mapembelo usiku ndi usana. 6Ata chimwecho, wamkazi yuja walama kwa chigololo afa ingakale wali moyo.7Ndi wavilakila ivi ilikuti asidakala ndi kukambidwa. 8Nambo ngati mundu siwasunga achabale wake, hasa waja ali mnyumba yake, waikana imani ndi oipa kuposa uyo siwavana navo.9Ndipo wamkazi walembechedwe muorodha ngati mjane wakale ndi vyaka ivyo sivipungua vyaka siitini, ndi wamkazi wanamuna mmoji. 10Mambo wakalewajiwika pavindu vabwino, ibidi kuti wasunga wana, pena watokala olemekekza kwa ulendo pena wasamba nywendo ya yao akulupi lilao, pena ikale watangatile yao amatesedwa, pena wadajichocha kwanjito iliyonje yabwino.11ambo kwawaja ujane anyamata, kana kwalembecha muoloza ya ajane pakuti akalowa mokumbila yakitupi poposa Kristo, afuna kukwatiwa. 12Panjila iyi alowe mu mmaeso pakuti atwola kujichocha kwao paoyamba. 13Ndi chocho alowa muchizowe tezi chaulesi anyiimwe azungulila nymba ndi nyumba opande pe kuti alesi, ndiposa osengenya ndi alindi kulowelela vindu vawina anyiimwe akamba vindu ivo sivakuza.14Ndipo imenifuna akazi anyamata akwatitwe, abale wane, aimilile nyumba zao pakuti asaninge oipa oipa mpata kutu manga vochita dhambi. 15Pakuti baadhi yao atokumngana mukila satana. 16Ngati wamkazi walionje wakulupilila ajane, ndiposo watangatile kuti kanisa sidalemekeledwa, kutilikaze kwatangatila wajaali ajane zene zene.17Ndipo midala waja aimililaobwino awelengedwe pakuti afai kulemekezedwa mala pangono, hasa waja ajituma ndi kuyaluza mau lamnungu. 18Pakuti malembo yakumba, "usidamasula ng'ombe pakamwa yapo wapuliza vauja," ndi "wachita njito wafunika malipilo yake."19Usidalandila madandauluzidi ya mdala kapena kuli madandaulo ingakale kuli mashaidi awili pena atatu. 20Akambe alakwa pamaso pawandu onje ili wina akala pena saope.21Ndutuma pauzene dhidi yapachogolo pa Mulungu, ndi pachogolo pa Kristo Yesu, ndi angelo osangidwa, kuti usunge ivo nakuagiza yaya bila chisackho chilichonje, ndi kuti usidita chindu chilichonje ko pendelea. 22Usida muikila mundu walionje manja kwa msanga usida ungana ndi dhambi ya mwina ifunika kujitunza umwene ukale bwino.23Sifunika kumwa majiweka, pambuyo pake, umwe mvinyo pangono pachifuko cha mmimba ndi matenda yako yandawi kwa ndawi. 24Dhambi zaochepa ya wandu ajiwikana pa uwazi, ndi kwachongolela muhukumu, nambo baadhi ya zambi ichata 25pambuyo.Chocho baadhi ya njito ya bwino ijiwikana pa uwzi, nambo atazina si zibisika.

Chapter 6

1Anyiwaja onche alipanchi ya achamunao, ngati akapolo atengele achamunao ngati ali niulemuanche, afunika kuchita chimwecho ilijina la Mulungu ndi mayaluzo siyadatukanidwa. 2Akapolo anyiyao ali ndi wachimuna aamini si adapepula kwa chifuko anyiio ni mabale. Pambuyo pake atumikile zaidi. Kwa chifuko wachimuna athangatilidwa nchito zao ni waamini ndi akondedwa kuyaluza ndi kuyatangaza vinthu ivi.3Ingakale munthu fulani wayaluza kwa kulakwila ndi siwayalandila maelekezo yantu yoaminika, ambalo ni mau la Ambuye wantu Yesu Kristo ingakale sialivomela yaluzo lichogoza munthu wa Mulungu. 4Munthu mmeneyo walindimalinga ndi siwajua chalichonche, pambuyo pake wali wananga ndikubishana pakti pa mau, mau yaya yabala nchanje, endeo malambunjo, , hisia yoipa. 5Ndi ndeo za nyengo kwa nyengo katika ya anthu ali ni njelu zowanangika aisia uzene ni njila yakukala.6Chipano siwaphe ndi kutizika ni faida yaikulu. 7Kwamate sitidaje ndi chalichonche pajhiko wala sitikoza kutenga chalichonche kuchokela pajhiko. 8Pambuyo pake tutosheke ndi vakudya ndi vovala.9Chipano anyiyao siakale ndi chuma, siagwe kupitila maeso, katika msampha saagwe kupitila uchile kwa wambili ndi tamaa yoipa, ndi katika chinthu chalichonche ichosichachite wanthu abile kupitila maangamizi ndi. 10Pakuti kukonda ndalama ni chanzo cha aina zonche voipa, wanthu ambao akhimbila imeneyo anyengedwa pathali ndi imani ndi ajilasa achinawenekwa.11Nampho iwe munthu wa Mulungu, yathawe mambo yamene chatha uaminifu, upendo usitahimilivu ndi upole. 12Ndikupacha matauko yaya pachogolo pa Mulungu uyo wachiticha vinthu vonche kulama ndiphachogolo pa Yesu Kristo, uyowadanena yali yauzene kwa Pontio Pilato.13Thimba nkhondo yabwino yamtendele gwililila umoyo wa milele uwowatanidwila idali ni kwa chifuko ichi kuti udachocha. 14Lituze lamulo kwa uzene, palibe mantha, hadi kubwela kwa ambuye watu Yesu Kristo.15Mulungu siwalangizile kuja kwake kwa nyengo ya uzene - Mulungu, abalikidwa, mphavu zayokha, mfumu uyowatawala, Mbuye yaotichogoza. 16Iyo yokjha walama muyaya ndi uyowakhala kupitila dangalila ilosilidakalibie, palibe munthu wakhoza kum,uona wala wakhoza kumpenya, kwake ikale ulemu ndi kukala wa muyaya.17Akambileni mafulu kupitila jhiko lino siadakhala nimalinga ndi siadakulupalila kupitila ufulu anyiyao osati auzene, pambuyo pake, afunika kumkhulupalila Mulungu ambaye watiphatila ufulu onche wa uzene ili thisangalale. 18Akambile achite vabwino, akale mafulu kupitila nchito yabwino, akale olandila, ndi. 19Kupitila njila imeneyo siajiikile msingi wabwino kwa vinthu sivije, ili kuti akoze kugwila maisha ya uzene.20Timotheo, penyelela chijha ichowapachidwa , jichoche ndi magwilizano yakipumbavu ndi malimba eneyochekeleza ambayo pakuti mtila utanidwa njelu. 21Baazi ya wanthu uyatangaza mambo yaya ndi chimwecho ailakwila chikulupi, neema ndi ikale pamoji nawe.

2 Timothy

Chapter 1

1Paulo utumidwa ndi Mulungu kwa chikondi cha Mulungu pamoji ndi kembidwe la mtendele ulimkati mwa Kristo Yesu. 2Kwa Timotheo mwane okondedwa ueneleli kulekeledwa ndimtendele kuchokela kwa Mulungu tate wake ndi Kristo Yesu olemakeze watu.3Ndimuyamika Mulungu mmeneyo ndi mgwilila nchito kwa mateyabwi no ngati umoadechitileanya ate tewanga, yapo mikumbukile ntawizoniche pamepemphelo yanga usiku na. 4Mchane ndikuambila kukuoneneni dala kuti ndikale ndi mtendele. 5Ndakala ndindikumbuchidwa pake tipa chikulupi chenechene chimene mmayambo chideli kwa ambuye aloisi ndi amanu Yunisi ndindi kuhupalile kuti chikulupi chi kale mkatimwako na we.6Ichi ndicho chifukwa ndikuku mbucha pano ya Mulungu ili mkati mwako kwa njila ya kuikidwila manja yanga. 7Pakuti Mulungu siwade kupache mtima wa manta ikapande mlima wa mpavu ndichikondi ndiulemu.8Kwaicho siodaona nchoni kukambilila nkani akondedwa watu inga kale ine Paulo umongidwa wake. 9Ndi Mulungu watipulumucha ndikuti tana kwa kutanidwa kwa bwino. 10Nampo chapamo upulumuchi wa Mulungu wa vunukulidwa chifukwa cha kuja kwa Yesu Kristo. Kristo ndimene wadasiicha nyifa ndi kubwelecho umoyo wosata kwa langizo la mau la Mulungu. 11Chifukwa kwa chimeneichi nidasa nkulidwa kukala mlaliki, otumidwa ndioyaluze.12Chifukwa chichi ndi chauchidwa cho nampo sindiona manyazi chifuko ndimjiwa mmeneyo nda mkurupalila. Ndili ndi uzene kutiiyeyo wako za kuchisunga chimene napachidwa kuchipeleka kwaiye ntawi imeneyo. 13Kumbukila langizo la utenga wa uzene wauvecha kuchokela kwaine pamoji ndi chikulupi ndi chikondi chili mkati mwa Kristo Yesu. 14Yasuage yali ya bwino wakupacha Mulungu kuchatila Mzimu Woyela ukala mkati mwatu.15Ujiwa kuti onche akala kuasia adandisia mkati mwao alimo Figelo ndi Hemogene. 16Mulungu wa ikurulukile nyumba ya Onesiforo chifukwa ntawi zambili zambili wadapeleka ubwino ndi siwada ionele manyazi vingwe vanga. 17Pambuyo pake pa mene wadeli kuhoma wada ndifunofuno kwa mbili ndi wadenipeze. 18Mulungu wamtandize kupeza kululiko kuchokela kwaiye siku limenalo ngati umo wa dandi tandizila yapo ndidali ku Efeso iwe ujiwa bwino.

Chapter 2

1Kwa icho iwe mwana wanga utilidwe mbhavu kwa lisungu ili lilimkati mwa Yesu Kristo. 2Ndi vicheto ivowavivela kwanga mkati mwa amboni ambili, uwapache wantu achilungamo yawo sakoze kuwayaluza wena nao.3Igwili zana mavuto pamoji ndiine, ngati msikari wa bwino mwa Kristo Yesu. 4Palije msikari wajichocha nyengo imweyo kujilovya ndi nchito zopepuka za ukalo uno, kuti ankondaweleche wa ulemu wake wapamwambe. 5Ngati muntu wake yambamila ngati otamanga siwa la ndila chisoti ngati osayambanile kochata molinga.6Ndi chamate kuti olima uyo wali olimbila wakale oyamba kulandila mkokolo wa vipacho vake. 7Ganizila chimene ninenacho pakuti ambuye siakupache kujiwa kwa vochitika vonche.8Mkumbukile Yesu Kristo kuchokela chibadwa Daudi uyo wadayhuka kuchokela kwa akufa. Ichi ni kulingana nidi utenga wanga wa ulaliki, 9umeneo cha odande ya uwo ndidavutichidwa mpakana kumangidiwa vichulo ngati olakwa. mampo mau la Mulungu losamangidwe kwa vichulo. 10Kwa icho ndidikila lawa vichito vonche kwa chifuko cha anyiwaja yawo Mulungu adatokuwasa ghai kuti naojiho nao apeze chipulumuchi chili kwa Yesu Kristo pamoji ndi ulemelelo usata.11Mau limelo ndi lokulupalika: "ngati tafa pamoji ndiiye, sitikale pamoji naye. 12Ngati sitidikilesitilamule pamoji ndiiye nampho tikamkana iye, nayencho siwatikane ife. 13Ngati sitikala olungama, iye siwakale wachilungama, pakuti siwakoza kujikana mwene".14Endekela kwakumbucha pakuti pa yaya. Wakambe pa maso pa Mulungu asiye akuchuchana kwa mau. Chifuno palibe chopata kwa nghani iyi kuchokana ndi ili kuli ndivowanangika lawa anyiwaje ovechela. 15Chiti chichimichimi kujilangiza kuti wavomelezedwa kwa Mulungu ngati ochita nchito uyo walije ndande ya kulaumidya. Lichitileni mau la usene lawa chilungamo.16Jichocheni ndi machuchano ya jhiko, yayo yachogozedwa nfi kupunda ndi kupunda ya panduka. 17Machuchano yao siyaenele ngati chilonda chosapole mumpingomwao ndi Himenayo ndi Fileto. 18Ayameneo ndi wantu yaoaulepela uzene. Akamba yakuti kutlyuka kudato chekela. Anglana muila chikulupi ya wantu akumoji.19Ata chimwecho msingi olimbikicha wa Mulungu waima, ndi ulembi uwu. "Ambuye wajiwa yaowaliwake ndi uyo walichula jina la ambuye wafunika wajipalule ndi zoipa". 20Mnyumba ya opata osati kuti vilimo vintu va dhahabu nsi shabape nampho kuti vintu vamitengo ndi doti. Vimojiwapo ya ivi ndi kwandande vena vyake kuvitumikila ko pande ulemu. 21Ikakala muntu wajichuka mwene kuchoka kuchitidwe loseti la ulemu, iye ni chintu cha kulemekezeka. Wapatulidwa yeka, ndi wamtengo kwa ambuye ndi walembedwa kwa nchito ya bwino.22Zitaweni zokadwilicha za unyamata. Muchate malinga chikulupi, chikondi ndi mtendele pamoji ndi anyiwajaauutana ambuye kwa mtima ochukika. 23Nampho ukane vaupumbafuu ndi mafujho ya chipuuli. Chifuko ujiwa yakuti yabala nghondo.24Otumika mwa ambuye siufunika kuyambana, pambuyo pake ifunika kukala ogodomala kwa wantu wonche wakoza kuyaluza ndi kudikila. 25Ndi chilungamo wayaluze kwa pang'ono pang'ono anyiwaja amchekeleza. Kapena Mulungu wakoze kumpachacholinga kwa kuiijino zene. 26Ukoze kupeza kujiwa pena ndi kujipepucha msambha wa satana, pamoji ya kuti watengedwa ndi iye kwa ndande ya chinondi chake.

Chapter 3

1Nampho ujiwe kuti kunsiku zotela kukale ndi nthawi zo limba. 2Ndande wanthu sakale ojikonda achinawene, akaleokonda ndalamu, akale ojielekela akale ajivuna. alije ulemu kwa makolo yao osajiwa kuyamika ndi opanduka. 3Alije chikondi cha mmayambo, Safune kukala kwa mtendele ni waliyonchhe, oyambanicha, onamizila, sakozi nujichekeleza, ali ndi ndeo, osakonda ya bwino. 4Sakale akupa, ambwinya, ojikonda achinewne, ndi okonda va jiko, osati kumkonda Mulungu.5Kwa kubwalo sakale ndinkhole ya kumjiwa Mungu, nampho saikane nkhongono yake. Kala kutali ndi wanthu achameneo. 6Pakuti wina wao ndi wachimuna alowa kumakamu ya wanthu ndi kwaguzi wachikazi owewela. Anyiyawa ndi wachikazi ajala machimo ndi anyi yao achoyozedwa ndi kumbilo za kila mtundu. 7Wachikazi anyiyawa ajiyatuze siku zonchhe, nampho sakoza kuliandikila kuijiwa ije zene.8Ngati umo uli yane ndi yamble adaima usalingano ndi Musa. 9Nampho saendekela patali. Pakuti kuwewela kwao, kukale kwa vunukulidwa kwe wanthu wonchhe, ngati umo udalu waanyiwaja wanthu.10Nampho iwe wayachata mayaluzo yanga, ndi njila zanga, kulupalilo langa, chikulupi changa, kuembeneza kwanga, chikondi changa, ndi kuvumilia kwanga. 11Mavuto mapwetekedwe ndi yayoyandipeza ku Antiokia, Konio ndi ku Listra. Ndidayaembekez mavuto. Ambuye adonipulumucha katika yonehheyo. 12Wonchhe afuna kukala katika umoyo wa kumjiwa Mulungu katika mpulumusi watu wavutichidwa. 13Wanthu oipa ndi onyenga siakale ndivolakwe vambili. Siwanomize ambili, achinewene anamizidwa.14Nampho iwe kala ktk vinthu wajifaluza ndi kuvikulupalila kwa mtima. Pakuti ujiw wajiyaluz kwa yani. 15Ujiwa kuli kuchoka kuumwana wako udayejiwe malembo yoela. Yaya yakoza kukupacha ulemu kwa kuomboledwa kwa njila ya chikulupi kwa mpulumusi.16Kila lembo lapachidwa umoyo ndi Mulungu, likwoma kwa mayaluzo ya pindu kwa kunyeng ndi kokonja volakwa ndikoyaluzil vabwino. 17Ili ndikuti munthu wa Mulungu wakale okamilika wakakala wapachidw nkhongono zonchhe kwa mate yochita kila nchhito ya bwino.

Chapter 4

1Nikupacha langizo lili nai kulemela pachogelo pa Mulungu ndi Kristo Yesu, uyo walamula yao amoyo ndi akufa, chifuko cha ndnde ya kuvunikulidwa kwo ndi ufumu wao. 2Lalikani mau. Ukali chonga kwa ntawi ya bwino ndi osati ya bwino wakambile wanthu machimo yao, kalipila, chisa ndi chiyembekezo chonche ndi mayaluzo.3Pakuti ntawi siije yapo watu satengelana ndi mayaluzo ya zene. Pambuyo pake, siajifunile oyaluza wa kuyaluza kulingana ndi makumbilo yao. Kwa njila iyi makutu uao siyakole yanyengelechedwa. 4Siasiye kuvelecha mayaluzo ya zene, ndi kung'anamukila mtano. 5Nampho iwe ukale wa chikulua kughani zonche, kuyembekeza yolimba, chita nchito ya ulaliki, maliza ulaliki wako.6Pakuti ine tayari ndato Pungulilidwa nyengo ya kuchoka kwanga wawandikila. 7Nambana chamalinga kaundedwe nakamaliza, chiyembekezo achisunga. 8Chisoti cha Malinga chikidw kwa chifuko changa, iyo ambuye, uyowalamul kwa malinga, siwanipache siku ija. Osati kwaine pe nampho kwa wonche omlindilila kwa kumbilo kuonekana kwake.9Limbikila kubwela kwaine msanga. 10Pakuti Dema wanisi. Walikond jiko la chipano ndi wapita Kuthesalonike, Kukreseni wadapita Kugalatia Ndi Tito wadapita KuDalmatia.11Luka tu ndiye wlipamoji ndiine. Umtenge Marko ujhe naye pakuti iye nde mate kwaine kwa ulafiki. 13Namtuma Tikiko ku Efeso. 12Lija joho ilo nidalisia ku Tro kwa Karpo, Yaposiuje nipelekle pamoji ndi vij vikalakala kupunda vija vya chikwetu14Alekizanda osula chichulo wadani chitila vuipa va mbili. Ambuye siambwezele kuchatana ndi vochita vake. 15Iwe nawe jipenyelele naye pakuti wadayachucha kupunda mau yatu. 16Pa chitetezo changa cha kuyamba palibe munthu waliyenche wadaima pamoji ndiine pamalo pake , kila mmoji odanisiya. Mulungu asadawelengela kulakwa.17Nampho ambuye adaima pamoji ndiine, adanipacha mphavu kuti kupitila kwaine, mau linenedwe kwa kukwanila ndi ajiko apeze kuvela. Nidapumuchidwa mkamwa mwa nkango. 18Ambuye sianipepeche ndi vochita vonche voipa ndi kunipulumucha chifuko cha ufumu wake wa kumwamba. Ulemelelo ukale kwa iye muya ndi muya. Amen.19Mlonjele Prisks, Akila ndi nyumba ya Onesoforo. 20Erasto wadakala ku Korintho, nampho Trifimo nidamsiya Kumileto wadali odwala. 21Chita msanga ubwele pa mbuyo pa ntawi ya mphepo. Eubulo wakulonjela. nayo pude, Lino, Claudia ndi abale wonche. 22Mulungu akale pamaji ndi mzima wako, lisungu likale ndi iwe.

Titus

Chapter 1

1Paolo Kapolo wa Mulungu ndi otumidwa a Yesu Kiristo, pa chikulupi chosankhidwa ndi Mulungu, ndi Malango yazene yopeleka kuyela. 2Alipo mchikulupi cha Umoyo osata, Mulungu osakoza kunena unami Chiyambile kale. 3Panyengo Adaluvunukula mau lake pa utenga uo mdanipachia kulalika, kuchita palamuo la Mulungu wathu.4Tito mwana wa uzene mkati mwa chikulupi chatu, neema, lisungu ndi mtendele kuchokakwa Mlungu atate ndi kwa Ayesu Kiristo Mpulumusi a wanthu. 5Pa ndande iyi ndidakusiya ku Krete uyakonde tonche yadalisiyada kwanilendi kuika wa akulu akulu anyumba ya mapemphelo pa muji ngati umo ndidakulamulila.6Wamkulu wanyumba ya mapemphelo asakala munthu odanda ulidwa, wa mmuna wakale ndi mkazi mmoji wali ndi wana okulupilika. 7Chachikulu openyelela, ngati oyimilila nyumba ya Mlungu, Wasakala odandaulidwa Wasakala munthu wa pokoso, Wasakala Munthu wamphwayi wasakala olojeda, Wasakala munthu oyambanichana, wasakala Munthu wakumbilo.8Pambuyo pake wakale munthu otanila. Wakale wa njelu zokwana, wakale okulupalila Mlungu, uyo wajisunga mwene. 9Wakoza kujimilila mayaluzo ya uzene yayoyayaluzidwa, kuti wakoze kwapacha mtima pamayakuzo ya bwina ndi wako ze kwa konja onche yao sakulupilila.10Pakuti kuli olakwa ambili, ndi mau yopande mate. Akunyengana ndi kwa chogoza wanthu kulakwa. 11Wanthu amtu uwu safunika ayuluza yosafunike pampotho ndi nchoni zao ndi ffamilia zonche.12Mmoji wao munthu wa ulemu wada kamba wa Krete ali ndi unami opande potela, oipa ngati zinyama zoluswa anchele ndi aludyo. 13Mau yaya ndi ya zene, wachekeleze kwa machili kuti akoze kukamba uzene ndi chikulupi.14Iwe usajilovyo hadith zo pande uzene za ayahudi15Pakuti onche abwino ndi vinthu vonche vabwino. Ndi kwa onche aliakuda, ndi osakulupalila, palibe, chilichabwino pakuti maganizo yao yadechedwa. 16Avomela kunjiwa Mlungu nampho vochita vao va akana, Anyuo ndi olakwa ndi alije ulemu. Saadatilidwe umboni pa la bwino lalilonche.

Chapter 2

1Nampho iwe uyakambe yayo yachatana ndi maelekezedzwe yokulupalilika. 2Midala akale ndi chipimo, ulemu, njelu, chikulupalilo cha bwino, kukala ndi chikondi kukala ndi kudikila.3Wachikazi okota naoncho, ajilangize achinawene ngati ali ojilemekeza, ndi aunami ndi sadakala akumwa mowa. 4Hunika kuyaluza ali ya bwino, ndikwakonja anamwali ulemu kwa konda aehamunao, ndi achana wao. 5Hunika kwayaluza. Kuti akale ndi ulemu akadwa ozikonja bwino nyumba zao, aulemu kwa chamunao, iunika kuchita nkhani izi kuti Mau la Ambuye lilemekezedwe.6Kwa mtundu umeneo mwapache mtima anyamata wachimuna akale ndi ulemu. 7Kwa njila zonehhe jiikileni mwaetima wene kukalao langizila kwa nchhito ya bwino yapo muyaluza, langizani kukala ndi ulemu. 8Kambanani utenga wa umoyo ulibe kulakwa kuti waliyonchhe wakamila waitidwe mwano ndande walibe loipa lokamba kwa ife.9Kapolo walemekeze bwana wake kwa kila komthuiyumika kwapacha, chisangalalo osati kulinga na ndi bwana wake. 10Sifumika kuba pamalo pake ifumika ahikulupi cha bwino, kuti kwa njila zonchhe wakadwiliche mayaluzo yatu yafuna Ambuye alamiche wanthu.11Pakuti neema ya Ambuye yaonekana ndi wanthu wonchhe, 12ituyaluza kukana nkhani iyo siili ya Ambuye ndi kukumbila vapajiko ituyaluza kukala kwa njelu, ndi kwa njila ya Mlungu kwa nthawi ino. 13Nthawi tifuna kulandila chikulupi ehatu cha daliso kuonekana kwa ulemelelo wa Mlungu watu wa mkulu ndi mpulumusi watu Yesu Kristo.14Mpulumusi wadachichocha mwene ntando wa ife kutuchocha kumachimo kukala oyela ndande yatu. Wanthu tifunika kuchita nchhito ya bwino.15Inene ndi kulimbikiza nkhani ii kalipa ndi kwa malamulo yonchhe, siudavomela Munthu waliyonchhe wakupepule.

Chapter 3

1Wakumbuche kwachikila ochogelela ndi ambavu, kwalolela ndi kukala chonga kwa nchito ya bwino. 2Wakumbuche osamchitile munthu watiyenche voyipa, atawe vyo kambi chana, awapache malo wantu wena kuchita malamulo, ndi vulangiza kuchika kwa wantu wonche.3Pakuti ie nae tidali ndi maganizo yotaika ndi mbwinya. Tidaipicha ndi kuipilana.4Nampho nyengo ya Lisungu la Mulungu mpulumuchi watu ndi chikondi chake kwa wantu yapo mdaonekana. 5Idali kwa vichito vatu vachilungamo ivyo tavichita ikapanda adatipulumucha kwa Lisungu lao. Adatipulumucha kwa kutichuka kubawa wa chipano kwa mzimu woyera.6Mulungu ada mwaza Mzimu Oyela opitiliha pamwamba patu kupitila Yesu Kristo Mpulumuchi watu. 7Adachita chimwechi kuti yapata welengedwa uzene ndi chikulupi chake tikale limoji ndi chikulupi cha ukalo opitiliha.8Uwo ndi utenga ovemeleka. Nikufunani muyaviambe lawa chimi chimi vichito ivi. Kuti anyamene maganizo pa mwamba pa nchito ya bwino iyo ayiika pachongolo pao. Vichito ivi ndi vabwino ndi ulemelelo kwa wantu wonche.9Nampho jipepucheni ndi mau ya kipumbavu. Yochuchana ya mpikisano ndi kupwanyana kuchatila lamlo. Vichito imenewo vitibe mate ndi uyeneleli. 10Mkaneni waliyenche uyowachiticha vigawo pakati panu. Pambuyo pa kukaniza limoji kapena ya wili. 11Jiwani kuti muntu wa mitundu imeneyo waisiya njila ya uzene ndi kuchita machimo ndi kuyilamulila wa mwene.12Yapo sinimtume kwa iwe Artemi kapena Tikiko, msanga ujhe kwa ine kuno kunikoli ndeyapo nalamula kukala nyenge ya mphepo. 13Chita msanga umtume Zena wakoza kulamula ndi Apolo pepande kuchepekedwa ndi chintu.14Wantu watu afumika ajiyaluze kujitandiza pa nchito ya bwino izo zifuna vofunika kuti osati adakale osabandwa vipacho.15Wonche yao alipamoji ndiine akulonjelani. Alonjele wonche atikonde pa chikulupi ndi mtendele vikala nanyi mwaonche.

Philemon

Chapter 1

1Paulo amangidwa nda ambuye mnungu, ndi abale Timotheo nda Filemon okondedwa abwenji watu ndi anchito palimoji ife, 2ndi kwa afela alongo watu, ni udande Arkipas ankondo achanjatu, ni udande nyumba ija ikomanika kukomo kwanga. 3Mwai ukale kwanu ni mtima uchokela ndande Amnungu baba wanga ndi ndande ya ambuye Yesu Krisito.4Nyengo yonche nimuyamika Mnungu nilichula pakati mapemphelo yanga. 5Nayavela ubwino ndi mtima uwomunao ndande ambuye ndi ndande ya wantu won. 6Nikupemmpani kuti chigwilizano ndi mtima yao ukweli chiuko cha chintu chikondi chilipo pakati panu nda Yesu. 7Pakuti ndidali nichisangalalo ndi ubwino wanu ndi pakuti mitima ya wantu ifdali imasi fidwa ndiiwe m-bale.8Pakuti udakakala nili ninchito wonche chikulupi cha ambuye kukulamulani imwe kuchita chija ichomukoza kuchita 9chifuko ni ndande ya chisangalalo, pambuyo pake ine, Pauli nidali mzee ndi chipano wamangindwa chiuko cha ambuye Yesu.10Nikuuza chifuko cha mwana wanga Onesmo, nidam-bala pamoji nikumangidwa kwanga. 11Pakuti mmayambo siwakutangatile nambo chipano wakutangatila iwe ndi inee. 12Namtuma iye pakuti ndi wa mtima wanga ndi kubwelakwanga. 13Nikulupalila wadakala kukala palimojindiine ili wanichitile badala yake nyengo nidali wako komangidwa chifuko cha mapembelo.14Pakuti sinidafune kuchita chidyu chalichonje popane malamulo yanu. Nidachita chimwacho ni mafuna chintu chalichonte chabwino sida chitika pakuti nidakulazimisha ndi pakuti udakonda umwene kuchichita. 15Kapina ndi pakuti wadasankidwa namulekwa unyengo idali chimwecho mukale naye palimoji naye milele 16ifunika kuti siwadakalancho otengedwa mmpo mbasa kupunda otengedua ngatiabale okondedwa.17Ni chimwecho unitangela ine oela, mlandile ngati chimwecho udakanilandila ine. 18Nambo ngati wanilakwila chintu chalichoche kapena umdai chimenocho kuchoka kwanga. 19Ine Paulo nilemba kwa janja langa namwene, ine sinikulipe, sinikamba kwako kuti nikudai maisha yako chipano. 20Ni amini m bale sia nifuna chisangalalo cha mnungu kuchokela kwanu; usangalaliche mtima wangu pamoji na ambuye.21Nikakala ndimtima kuchita sala zanu nikule mbelani nikajiwa kuti sinichite zaidi vija umonipembelani. 22Nyengo imeneyo uandue chipinda cha alendo kwa udande yanga pakuti sinikulupalile kupitila mapemphelo yako sinikuendele saa imweino.23Epafra, amangindwa anjanga pamoji na Akristo Yesu akulonjela. 24Ningati umouchitia Marko, Aristarko, Dema, Luka, Anchito pamoji ndiine. 25Chisangalalo cha ambuye Yesu Kristo chikale pamoji ndi mtima wanu. Ame.

Hebrews

Chapter 1

1Nyengo zopita Mulungu wadakambana ndiacha Ambuye wathu kupitila olosa ala kambili ndi wa njla zabili. 2Nampo pakati pa siku izi tili nazo, Mulungu wakambana nafe kupitila mwana, uyo wadamwika kukhala kuti osiidwila wa vinthu vonche, ndi kpitila iye wadalikonja jhiko. 3Mwana wake ni dangalila la ufulu wake, khalidwe la palokha la asili yake, ndi waendekela vinthu vonche kwa mau la mphavu zake. Pamalo pokwanicha kuchukika kwa machimo, wadakhala panchi janja la kwene ndi la enzi kumeneko kumwamba.4Wali bwino kupitilila angelo, ngati mujha jhina ilowada siidwila umo lilibwino kupitilila jhino lao. 5Kwa mathe ni kwa angelo yuti wadachogola kukamba, "iwe ni mwana wanga, lelo nili tate wako?" Ndi tena, "sinikhale tatewako, nae siwakhale mwana kwanga?"6Tena Mulungu yapo wadampeleka obadwa oyamba pajhiko, wadakamba, angelo onche a Mulungu lazima akutamande. 7Kukhuza angelo wakamba, "iyeuyo wachita angelo wake kukhala mzimu, ndi atumiki wake kukhala ngati ndimi za moto."8Nampho kukhuza mwana wakamba, "mpando wako wa enzi, Mulungu ni wa muyaya ndi muyaya. Mpulu wa ufumu wako ni mpulu wa haki. 9Wakonda haki ndi kuipila kutyoledwa kwa thauko, kwa chimwecho Mulungu, Mulungu wako, wakupaka mafuta ya chisangalalo kupitilila achanjako."10Yapo poyamba, Ambuye adaika msingi wa jhiko mitambo ni nchito za manja yako. 11Sizichoke, nampho iwe siwendekele. Zonche sizichakae ngani vovala. 12Siupindepinde ngati koti, nazo sizing'anamuke ngati vovala, nampho iwe ni mmweyujha ndi vyaka vako siilapa."13Nampho ni kwa angelo yuti Mulungu wadakamba nyengo yaliyonche, "kala jhanja langa la kwene mbaka yapo sinichite oipa wako onche kukhala mpando wa myendo yako?" 14Bwa, angelo onche opande mizimu iyo idatumidwa kuwathandiza ndi kuwasunga anyiwajha saasidwile kuomboledwa?

Chapter 2

1Kwachimwecho ni lazima tiike kipaumbele zaidi kwa yaja tayovela, ili kuti sitidaja kusankhidwa patali nayo.2Kwa chifuko ikakala khani iyoyakambidwa ndi angelo ni halali, ndi kila cholakwa ndi kulandila adhabu tu. 3Sitipate bwanji kujiepusha ngati sitilandila chilanga ichi chachikulu? Chilanga ambacho kwazachidatangazidwa ndi Ambuye ndi kusibitisha kwathu ndi anyiwajha adauvela. 4Mulungu nayo wadasibitisha kwa ishara, aajabu ndi kwa vichito vavikulu patali patali, ndi kwa mphaso za Mzimu Oyela izowadazigawa kulingana ndi mapenzi yake mwene wake.5Mulungu siwadaiike jiko likuja, ambapo tikambililila nkhani zake, phanji pa angelo. 6Pambuyo pake, munthu fulani washuhudia pamalo fulani niwakamba, "munthu ni yani hata ukoze kumkumbukila? Au mwana wa munthu, atawampenyelele?7Wamchita munthu kukala wamng'ono kuliko angelo; wamveka taji ya ulemelelo ndi ulemu. (zingatiani: mau yaya ndi wamuika pamwamba pa nchito ya mana yako yalibe kunakala za kale). 8Waika kila chinthu panchi pa myendo yako, kwa chimwecho Mulungu waika kila chnthu panchi pa munthu, siwadasie chinthu chalichonche sichidali panchi pake. Nampho chipano saino siwationa wakali kila chinthu chikakala panchi pake.9Ata chimwecho, tiona uyowadali wachitidwa kwa nthawi, panchi kuliko angelo Yesu uyo, kwachifuko cha mateso yake ndi nyifa yake wadavekedwa taji ya oela ndi ulemu. Chimwecho chipano kwa mwai wa Mulungu, Yesu walaw nyifa kwa chifuko cha kila munthu. 10Idali bwino kuti Mulungu, kwa chifuko kila chinthu chili kwa chifuko chake ndi kupitila iye wadafunika kwapeleka wana ambili kupitila chitukuko, ndi kuti wadafunika kumchita olamul kupitila uwokovu wao kukala okamilika kupitila mayeso yake.11Kwa mate onche awili yuja waika nchanje ndiwaya ambao aikidwa nchanje onche achoka kuasili imoji, Mulungu. Kwa chifuko ii yuja waika nchanje kwa Mulungu siwaona nchoni kwaatana abale. 12Wakamba, "sinitangaze jina lako kwa mabale zanga, siniimbe kuhusu iwe kuchoka mkati mwa gulu."13Tena wakamba, "siniamini kupitila iye," ndi tena, "penya, pano nili ndi wana ambao Mulungu wanipacha." 14Kwachimwecho, pakuti wana wa Mulungu onche ndikugwiliza thupi ndi mwazi, kadhalika Yesu wadagwiliza vinthu vivija, ili kuti kupitila nyifa wapeze kumdhoficha yua ambaye wali ni mlamulo pamwamba ya mauti, ambayo ni satana. 15Ii idali chimwecho ili awaike huru anyiwaja onche ambao kupitila mantha ya kufa adakala maisha yao yonche katika ukapolo.16Kwa hakika osati angeo uyowatandiza pambuyo pake, watangatila ubadwa wa Abrahamu. 17Kwachimwecho, idali lazima iye wakale ngati abale wake kuptila njila zonche kukala kuhani wamkulu wali ndi lisungu ndi oaminika kwa vinthu va mulungu, ndi il kuti wakale ndi uwezo wa kuchocha msamaha kwa machimo ya wanthu. 18Kwa chifuko Yesu mwene wateseka, ndi kuyesedwa, wali ndi uwezo wa kuwatangatila waja ayesedwa.

Chapter 3

1Kwaicho abale oyera, mwatanidwa kumwamba, mganizeni Yesu, mtumi di wa mkulu wa nchembe wachikuluplila chatu. 2Wadali wokhulupilika kwa Mlungu iye wadamsankha, ngati Musa umo waliokhulupirika naye mkati mwa nyumba yonche ya Mlungu. 3Pakuti Yesu wawelengedwa kukhala ndi ulemu wa mkulu kuposa nyumba yene. 4Pakuti nyumba yaliyonche imangidwa ndi munthu wakutiwakuti. Nampho uyo wamanga chinthu chilichonche ndi Mlungu.5Musa wadali okhulupirika mnyumba yonche ya Mlungu ngati wanchito chabe, wamachocha umboni pakati paizo sizioneke mchogolo. 6Nampho Kristo ndi mwana pakati pimilila nyumba ya Mlungu.Ife ndi nymba yake ngati sitigwililile mwamsanga pakati pjikulupirila ndi kulimba mtima.7Kwaicho ngati mzimu oyera umo ukambila, lelo ngati siuvele mau lake. 8Usachita mtimawako kukhala olimba ngati Aisraeli umo adachitila pakulakwa, pa nyengo ya maeso mpululu.9Ni idali nthawi acha atate wanu adandila kwila pakundiyesa, ndi nthawi, pa viaka makhumi ya nai, adaona vichito vanga. 10Kwaicho sindidavikondwele vibadwa vimenevo. "Ndidakamba, nyengo za mbili ataika mitima yao ndisazijhiwa njnila zanga. 11Ngati umo ndidalumbilila mwamphwayi zanga salowa mchisangalalo changa."12Khalani maso, Abale kuti usakhalapo mtima oipa osakulupilila mkatikati mwanu. Mtima uwo siukhale patali ndi Mlungu wa moyo. 13Pambuyo pake mjilimbikichana masik yonche mwina ndi mwina, kuti yapo ikala lelo mikhumbila, kuti mmoji wanu wasachitidwa kukhala olimba ndi chinyengo cha machimo.14Pakuti tili limoji ndi Kristo ngati tiagwilana ndi kulimba mtima kwathu kwa mphamvu mkati mwaiye chiyambile mmayambo mbakana mmathelo. 15Pakati pa ili latokambidwa lelo, "ngati mkalivela mau lake, msachita mitima yanu kukhala yolimba, ngati Aisraeli umoadachitila panyengo ya kuchimwa."16Ndi achiyani anyameneo adamvela Mlungu ndi kulakwa? Sadali anyiwaja onche wada achogoza Msa kuchokela ku Misiri? 17Nde achiyani yawo Mlungu wadaakwiila viaka makumi ya nai? Osati pamoji ndi anyiwajha achita machimo, yawo mathupi yao yadafa ndikugona mphululu? 18Achiyani wadalumbila Mlungu kuti salowa mkati mwa chisangalalo chake, ngati osati anyiwaja sadamvele iye? 19Tiona kuti sadakoze kulowa mchisangalalo chake ndande sadakulupalila.

Chapter 4

1Kwa icho, tifunika kukala chonga kuti pakati panu wasakalapo mmoji wanu kulepela kupeza pumililo la Mlungu. 2Pakuti utenga wa bwino walaliidwa kwatu ngati umo udalalikidwa kwa Aisraeli, nampho utenga siudatangatila chilichonche, pakuti adauvela nampho saadaulandile mwa chikulupi.3Ife tikulupilila tipeza mpumililo umene walonjeza Mlungu ngati umo wadakambila, nidakwia ndi kulapila salowa pamalo panga popumilila, Mlungu wadakamba yameneyo ingakale nchito yake idatokuta chiyambila yapo wdalenga jiko la panchi. 4Pakuti malembo yakamba Mulungu wadapumilila siku ya saba, wadasiya nchito zake zonche. 5Kenaka, yalembedwancho "saalowa pamalo panga popumilila."6Kwa icho yolowa ikalipo, pakuti anyiwaja adalalikidwa kale utenga wabwino, adapeleka kulowamo ndande adalibe ulemu. 7Mlungu wadaika siku lina litanidwa lelo, pambuyo wadakamba kwa njila ya Daudi mau yayo yadato chulidwa , ngati mkavela Mlungu wakamba lelo, msakala ndi mbwinya.8Ngati Yoshua wadakali waapacha wanthuo mpumililo, Mlungu siwadakamba kwa siku injake. 9Kwa icho kukalipo kupumulila kwa wanthu a Mulungu. 10Mate yake, kila uyo walowa mu mpumililo wa Mlungu siwapumilile pa nchito zake ngati Mlungu umo wadapumilila pa nchito yake. 11Kwa icho tilimbikile kulowa mu mpumililo umeneo kuti wasakalapo mkati mwatu uyo siwakane ulemu ngati umo adachita anyiiwo.12Mau la Mlungu la moyo, ndi lili mphavu, lidula osati ngati chikwanje chidula ukundi uku, ndi libucha ndi kupalulicha mtima ndi mzimu ndi vifwalo ndi mafuta ndi likoza kujiwa maganizo ya mtima. 13Palibe icho chalengedwa chibisika pamaso pa Mlungu kila chinthu chavunukulidwa kwa iye wali ndi kila chinthu tilinacho ifa.14Pambuyo tili nae wamkulu wa nchembe walowa kumwamba, Yesu mwana wa Mlungu, kolimikila tigwililile chikulupi chatu. 15Uyu wamkulu wa nchembe yu wajiwa mavuto yatu, mwene wadayesedwa ndi mdani, ngati ifa kwa kila mtundu nampho siwachite machimo. 16Kwa icho popande mantha tiusendelele mpando wa Mlungu wa mwai, tilandile lisungu ndi mwi olitangatila nyengo ya mavuto.

Chapter 5

1Kwai vila wamkulu wa nchembe, uyowasagulidwa kuima pamalo pawo mwa vindhu viwandikizana ndi Mulungu, mbhaso ndi nchembe kwa chifuko cha machimo. 2Wakoza kujhuichiticha kwa kujichicha ndi kupusa ndi ochucha pakuti iye mwene naye wazungulilidwa ndi kulepeledwa. 3Kwa ndande yayili waliofunika kwa kuchocha nchembe kwa chifuko cha machimo yake ngati lemowachitila kwa machimo ya wandhu.4Ndi palibe mundhu watenga ulemu uwu kwa chifuko chake mwene, namphjjo pamalo pake, lazima watanidwe ndi Mulungu, ngatilemu wali Haruni. 5Ata Kristo siwadajhipache ulemumwene kwa kujhichita mwene kukala wamulu wa nchembe. Pamalo paqke, Mulungu wadanena kwaiye, "iwe ni mwanawanga, lelo nakala atate wako."6Nde ngati umoanenelancho pamalo pena, "iwe ndi wanchembe osata pambuyo pa kalidwe la Melkizedeki."7Nyengo ya ntawi mwa tupi adapembha, ndi kupembhela adampembha Mulungu kwa misosi, kwa iye wakosa kumlamicha kuchokela ku nyifa. Kwa ndande ya kujichicha kwake kwa Mulungu wadaveledwa. 8Ingakale wadali mwana, wadajiyaluza ulemu kwa vichito vidamphweteka.9Wadakwanichidwa kwa njila iyi wadachitika kwa kia mundhu wamkulupalila kukala ndande ya chipulumuchi chosata. 10Kwa kupatulidwa ndi Mulungu ngati wamkulu wa nchembe pambuyo pa zamu ya Melkizedeki. 11Tili ndi ya mbili ya kunena kukuza Yesu nampho ndi kulimba kukukambilani pakuti anyiimwe ndi alesi wakuvela.12Pamojhi ndi kuti kwa ntawi iyi mdafunidwa kukala opunzila, kukati malo ya mundhu kukuyaluzani mayaluzo ya mmayambo kwa ntundu wa mau la Mulungu mfuna likama osati chakudya chakulama. 13Pakuti waliyenche wakumwa likama pa walijhe kuzowelala mwa utonga wa malinga pakuti wakali mwana. 14Kwa bendeka lina chakudya cholama ndi cha wandhu wakulakulu, anyiwajha yano kwa ndande ya kuzowelela mwa kusintanichan malinga ndi kuipa ayaluzidwa kujhiwa labwino ndi loyipa.

Chapter 6

1Chocho, tikasiya ichotajiyaluza kuusu utenge wa Kristo, ifunia kukala ndi kujituma kupita kukukwima , sitidaikajo misingi yochilisidwa kuchoka panjito zisili zolama ndi mtendele pa Mulungu, 2wala misingi yoyaluzidwa ya tiliwa a maji ndikukwaikila manja, kuzuchiwa kwa akufa, ndi chilango ha muyaya. 3Ndi sitichite ichi ikakala Mulungu siwatiluhusu.4Pakuti sikozekana kwaja adapata nulu mmayambo yao adalawa mbavu zakumwamba, ndikuchitidwa kukala okondedwa aloho oyela. 5Ndiyao adalawa ubwino wamau la Mulungu ndi kwavu za ndawi ikuja. 6Ndiposo adagwa - sikozekana kwabweza njo pakati patobna iyi ndi pandande ya amsulubicha mwana wa Mulungu mala ya kawili panafazi zao, ndikumchita kutichinda chokumdelela pa wazi.7Pakuti ndaka iyoidalandila vula ikunya ndawi zoje pamwamba pake ndi kuchocha chakuja chabwino kwa yao apota njito pandaka, kulandila mboto kuchoka kwa Mulunu. 8Nambo ikale ibala minga ndimauju, ulibejo samani ndi ili pachimbekezo cho laanidwa mmatelo mwake ndi kubuchidwa.9Ingakale tikamba ichi, mbwenji okondedwa, tikambidwila ndi vindu vabwino yahusuyo anyiimwe ndi yahusu kuokoka. 10Pakuti Mulungu opande zalimu ata waiwale njito yatu ndi pachikondi mudalangiza pajina lake, pakati pailimutatumikila au naini ndi mukali kwatumikila.11Ndi tikumbila kupunda kuti kila mmoji moji wanu wakoze kulangiza bidii iifa mbaka mmatelo pauwakika wa ujasili. 12Sitifuna mukale alesi, nambo mulale afuasi alidhi hadi pande ya mtendele ndi kuvumiliya.13Pakuti Mulunu yapo wadamnikha abhahemu chenjezo, wadalumbila panafasi yake, pakuti siwadalumbila kwa mwina waliuje wali wakulu kuposa iye. 14Wadakamba, "uzene sindikubaliki, ndisikuongezele chibadwa chako kupunda." 15Panjila iyi,Abrahamu wdalandila chifa wadakamidwila baada yolindila kwa kuvumiliya.16Pakuti wandu kulapa kwaiye wali wamkulu kuposa iwo, ndi kwao mmatelo moshindana vonje kulapa kwao kuyalimbikicha. 17Pandawi Mulungu yapowadalamula kulangiza pawazi kupunda koolisi aahadi ndande yake labwino ilosili sindika, wadasibitisha kwa lumbilo. 18Wadachita chocho kuti pvindu viwili ivosivikoz kusindika, ambavo pakati pavimene Mulungu siwakoza kukamba mila, ife tidantamangila malo tipeze kutilidw moyo kugwililila kwa mbavu chibekezo chidaikidwa pachongolo patu.19Tilinao ufasili uwu ngati nanga yolama ndiya kukulupilila mitima yatu, ufasili uli ulosa mkati kubwalo kwa paziya. 20Yesu wadalowa malo mmene ngati mchongoleli watu wakuta kuchitika kuhani wakulu ata muyaya pambuyo pa kukonjeka kwa Melekizedeki.

Chapter 7

1Idali mchimwe Melkizedeki, mfumu wa Salemu, wanchembe wa Mulungu wali pa mwamba, uyo wapezna ndi Abrahamu ndi wabwela kuchoka kwa oipa mafumu ndi wadambariki. 2Abrahamu wadamnikha imaji ya kumi ya kila chinthu icho wadachiteka, jina lake "Melkizedeki" maana yake "mfumu wa malnga" ndi "mfumu wa Salemu" ambayo ndi "mfumu wa mtendele." 3Walibe atate, walibe akumbala, walibe kuyamba kwa siku wala kuthela kwa maisha yake. Badala yake, wakala wa nchembe wamuyaya, ngati mwana wa Mulungu.4Chipano ganizila jinsi uyu munthu umawalima mkulu utubala wathu Abrahamu wada mnikha imojhi ya kumi ya vinthu vabwino ivowadatonga kunkhonda. 5Ndi uzene, ukoo wa Walawi anyiyawo adalandila mboma za anchembe adalindi lamulo kuchakakwa waizilaeli achanjao, pamoja ndi kuti anyiiwo, ncha, ndi ukoo kuchoka kwa Abrahamu. 6Nampho Melkizedeki, uyo siwadali wa ukoo kuchoka kwa Walawi, wadalandila imoji ya kumi kuchoka kwa Abrahamu ndi wadambariki, iyewadalindi ahadi.7Pamenepo sikanidwa kuti munthu wang"ono wambarikidwa ndi wamkulu. 8Kwa chichita ichi munthu uyowalandila imoji ya kumi siwafe siku limoji, nampho kwa chichita chinancho mmoji uyowalandila imoji ya kumi kwa Abrahamu idaelekedwa ngati uyowaishi. 9Ndi kwa namna ya kukamba, Lawi uyowalandila imoji ya kumi, ncho wadalipa imoji ya kumi kwa Abrahamu. 10Chifukwa Lawi wadali pakati pa viuno va atate wake Abrahamu nyengo Melkizedeki yapowadapezana ndi Abrahamu.11Chipano ngati uzene udakozekana kupitila anchembe wa Walawi, (mchimwecho panchi pake wanthu alandila lamuro), kudali ndi uitaji wanji laidi kwa wanchembe mwina kuinuka baada ya mfumo wa Melkizedeki, ndi osati kutanidwa baada ya mipangilio ya Haruni? 12Chipano wanchembe wakabadilika, palibe budi lamuro na la kubadilika.13Kwa mmoji ambaya vichito ivi vidakambidwa kuhusu kabila lina, kuchoka kwake palibe uyo wadahudumu pa mazabao. 14Chipano ndi obala kuti mbuye wanthu wadachoka pakati pa Yuda, kabila ambalo Musa siwadataje khusu anchembe.15Ndi yaya tukambandi wazi hasa ikakhala wanchembe mwinancho siwachokele kwachifani cha Melkizedeki. 16Wanchembe uyu wampya osati mmoji ambayo wali wanchembe pamwamba pa msingi wa lamulo izo zihusu ndi chibadwa cha wanthu, nampho kupitila msingi wa mphavu ya maisha yayosiyakoza kuwanangika. 17Mchimwecho malembedwe yalangizila kuhusu iye, "iwe ndi wanchembe wa muyaya baada ya mfumo wa Melkizedeki."18Pakuti ramulo ili lidachogolela lidaikidwa pamphepete kwa chifukwa idali dhaifu ndi simafai. 19Mchimwecho ramulo sidachite chalchonche chazene ingakale, kudali ndi ujasili wa bwino kwa yameneyo tumsendelela Mulungu.20Ndi ujasiri uu wa bwino siudachokele bila kukambilila kulapa kwa ili anchembe wina siadatenge kulapa kwa chalichonche. 21Nampho Mulungu wadatenga kulapa nyengo yapo wadakamba kuhusu Yesu, "mbuye walopa ndi siwabadilisha maganizo yake, iwe ndi wanchembe muyaya."22Kwa ili Yesu ncho waja kukala dhamana ya kuvamelezana kwa bwino. 23Kwa uzene nyifa yazuia anchembe kuhudumu kwa muyaya ii ndi kwa chifukwa adalipo anchembe ambili, mmoji baada ya mwinancha. 24Nampho kwa chifukwa Yesu waishi muyaya wa nchembe wake siubadilika.25Chipano iye ndo wakaza kwa uzene kukamilicha kwa lamicha anyayawo amsendelela Mulungu kupitila kwake, pakuti iyewaishi nyengo yonche kwa kupempha kwa chifukwa chao. 26Chipano wamkulu wanchembe wa namna ii wastahili kwathu, walibendi vochimo,hatia, msafi, uyowaikidwa pamphepete kuchoka kwa achima, ndi wali pamwamba kuliko kumwamba.27Iye siwadali ndi kufuna, chifanizi cha wakulu anchembe kuchocha nchembe kila siku, mmayambo kwa vochima vake mwene, ndi pambuyo pake kwa vochimo vawanthu wadachita mchimwechi kwa mala kamoji kwa anche, yapowadaji chacha iye mwene. 28Kwa ramulo wasakhula wanthu dhaifu kukala wakulu anchembe, nampho maula kulapa, lidaja. Baada ya ramulo, wadamsakhula mwana, uyowadachitidwa kukala wazene muyaya.

Chapter 8

1Chapano nkani imeneyo tikamba ndi iyi yilinaye busa wa mkuru wakala panchi pakati janja la kwene wa pampando wa ulemu wosata kumwamba. 2Iye ndi mtumiki pakati pamalo ya bwino, paloyokomanila ya zene limeneMulugu waliika osati muntu waliyenche womwalila.3Chifuko busa waliyenche wa mkuru waikidwa kunchocha mpaso ndi maya niko kwa mmwemo ili ndi mate kukala ndi chintu chochocha. 4Chapano ngati, Mkristo wadali pamwamba pa jiko iye ngati siwadakakale busa kupunga kwa pamenepo. Pakuti adali chika lilije anyiwaja adachocha mpaso kuchatana ndi malamulo. 5Adatandizila chintu chimene chidali nkope ndi chizindi kililo cha vintu va kumwamba kulingana ngati Musa wadalamichidwa nyengo ndi wafuna kuwanga pamalo po komani penyani Mulungu wadakamba kuti konjani kalikonche kuchatana ndi malunjidwe udelangilichwa kumwamba kwapili.6Nampo chapano Kristo walandila tandizidwe na bwino kupunda chifuko iye nayenche ndi okonchechana wavemelezedwe labwino, limene lato kuimililidwa kwa pangamo la Mulungu labwino. 7Mmwemo ngati pangano loyamba filida kakalapo ndi kulakwa ndi pamenepo sipadeka funika kukalapo ndipangano la kawili.8Pakuti ntawi Mulungu yapo wadajiwa volakwa va wantu wadakamba, "Penyani masiku yalimkuja" wadakamba Mulungu ntawi ndini konja pangano la chapano ndi nyumba ya Iziraeli ndi nyumba ya Yuda. 9Silikala ngati pangano likale ndianya atate wao ntawi imeneyo ndita watenga kwa manja kwa achogoze kuchokela Kumisiri. Chifuko siado endekele pakati pa pangano langa nanencho sindi ola atengelelencho, wakamba Mulungu.10Pakuti ilinde pangano silichitika munyumba ya Iziraeli pambuyo pa masiku yameneyo, "wakamba Mulungu" sindiike lamulo langa mmaganizo mwao ndi sindizilembe mmitima mwao, sindikale Mulungu wao naoncho siakale wantu wangu.11Sayaluzane waliyenche ndi pafupi naye ndi waliyenche ndi mbalewake ndi akamba, "mjiwe Mulungu mmwemo wonche siandijiwe ine, kuchokela wa mng'ono mpakano wa mkuru wao. 12Mmwemo sindilangize kuleketela kwa vichito vyao vilije ubwino ndi sindiyakumbukila machimo yao."13Pakkamba, "poyambila" walichita pangano loyambakukala lalikuru ndi ili limene walilengeze kukale lalikulu lilachitika kuchoka.

Chapter 9

1Chipano ata kuvomelezana koyamba kudali ndi malo yo pemphela pano pajhiko ndi kupenyelela kwa kupemphela. 2Ndi pakati pa hema padali ndi chumba chakonjewa, chumba cha kubwalo patanidwa pamalo poela. Pakati pa malo yaya padali ndi pothela pa nyali meza ndi mikata yalangizila.3Ndi kumbuyo kwa panzia kudali ndi chmba chinjake, patanidwa pamalo poela kupunda. 4Yadalimo mazabau ya zahabu yafukizia uvumba tena lidalimo bakosi la kuvomelezana, ilo lidali lamangidwa kwa zahabupe. Mkati mwake mudali pakuli la zahabu la mana, mpulu wa Haruniuo udamela wachamba, ndi yajha matabwa ya kuvomelezana. 5Pamwamba pa bakosi la kuvomelezana maumbo ya maserafi wa ufulu avinikila mapapiko yao pachogolo pa mpando wa kuvanichana, uo sazino sitikhoza kuukambilila kwa mkati.6Pamalo pa vinthu ivi vathokonjedwa, makuhni ku nthethe aloa chumba cha kubwalo cha hema kuchocha mthandizo wao. 7Nampho kuhani wamulu walowa chijha chumba cha kawili yokha mala kamojhi kwa chaka ndi popande kusiya kuchocha zabihu kwa chifuko chake yokha, ndi kwa machimo ya wanthu yayoadachita popandekujhiwa.8Mzimu oyela uchimikiza kuti, njila ya pamalo poela kupunda ikali yosamasulidwe kwa ndande hema loyamba likali chiimile. 9Ichi ni chifanizi cha nyengo ino ya chapano vonche mphaso ndi nchembe ivo vichochedwa chapano sivikhoza kukwanicha ganizo lauyo wamgwadila. 10Ndi vakudya ndi vakumwa vaphanikizidwa pakati mtundu pa khalidwe la ibada ya kujhichuka. Vonche ivi vidali khalidwe la thupi ivovidali vakonjedwa mbaka lijhe thauko la chapano ilo siliikidwe pamalo pake.11Kristo wadajha ngati Kuhani wa mkulu wa vinthu va bwino ivovajha kupitila ukulu ndi kukwanila kwa hema ya ikulu iyo siidachitiw ndi manja ya wanthu, io opande wa jhiko lino ilolaonjedwa. 12Idali opande kwa mwazi wa mbuzi ndi ndama. Nampho kwa mwazi wake mwene kuti Kristo wadalowa pamalo poela kupunda kamojhi kwa kila mmojhi ndi kutichimikizila kuomboledwa kwathu kwa muyaya.13Ngati kwa mwazi wa mbuzi ndi mafahari ndi kunyunyizilidwa kwa nyoso va ndama pakati pao opande oela adasankhidwa kwa Mulngundi kuchita matup yao bwino. 14Bwa opande kupunda mwazi wa Kristo iye kupitila mzimu wa muyaya wadajichocha mwene popande mawaa kwa Mulungu, kuchuka maganizo yathu kuchoka vichito mafu kumtumikila Mulungu wali wa moyo? 15Kwa ndande imeneyo, Kristo ni mthenga wa kovomelezana kwa chapano, ii opande ndande nyifa yasiye huru onche ali ovomelezana oyamba kuchokela pakati pa machimo yao, kuti onche atanidwa ndi Mulungu akhoze kulandila chilang chosiidwila cha muyaya.16Ngati kuli kuvomelezana kulama, ni lazima kuthilila umboni nyifa ya munthu yujha wadachita. 17Kwani kuvomelezana kukhala ndi mphavu pamalo pachokela nyifa, kwa chifuko palijhe mphavu nyengo mwene kulichita wakhala walama.18Chimwecho ata opande kujha kuvomelezana koyamba kudaikidwa popande mwazi. 19Nyengo Musa yapo wadachocha kuvomelezana kwa thauko kwa wanthu onche, wadatenga mwazi wa ng'ombe ndi buzi, pamojhi ndi majhi, chitambaa chofuwila, ndi hisopo, ndi kwanyunyuzila gombo lene ndi wanthu onche. 20Ndo wadakamba, uu ndi mwazi wa kuvomelezana uwo Mulungu wapacha thauko kwao.21Pakati pa khalidwe limwelijha, wadanyunyizila mwazi pamwamba pa hema ndi vinthu vonche ivo vidatumka kwa mthandizo wa anchembe. 22Ndi kulingana ndi thauko, pafupi kila chinthu chichukidwa kwa mwazi. Popande kumwaza mwazi palibe kulekeleledwa.23Kwachimwecho idali lazia kuti nakala za vinthu va kumwamba lazima vichukidwe kwa ii nchembe ya vunyama. Ata chimwecho, vinthu va kumwamba vene vidafunika kuchukidwa kwa nchembe idali ya bwino kupunda. 24Kwani Kristo siwadalowe pamalo poela kupunda yapopadachitidwa ndi manja, icho ni nakala ya vinthu vazene. Pambuyo pake wadalowa kumwamba kwene, pamalo yapo wali sazino pachogolo pamaso ya Mulungu kwa chifuko chathu.25Siwadalowe kujha kwa chifuko cha kujhichocha nchembe kwa chifuko chake mala kwa mala, ngati umowachitila wanchembe wankulu uye walowa pamalo poela kupunda chaka pabuyo pa chaka pamojhi ndi mwazi wa mwina. 26Ngati imeneyo idali zene, basi idakakhala lazima kwake kuzunjika mala za mbili kupunda kuyambila poyamba pa jhiko. Nampho saino mala kamojhi hadi pothela pavyaka umowada jhimasulila kujhichocha machimo kwa nchembe yake mwene.27Ngati umo ili kwa kila munthu kufa mla kamojhi ndi pamalo pa limenelo likujha laamulo. 28Nde n'chimwecho Kristo nae uyowadachochedwa mala kamojhi kuyachocha machimo ya ambili, siwachokele mala yakawili, opande kwa dala la kushughulikila machimo, popande kwa kuomboledwa kwa wajha amlindilila kwa saburi.

Chapter 10

1Kwa chijha lamulo ni mtunchi wavinthu vabwino yakuja, osati yaja yadali halisi, lamulo basi siikoza kuwakamilisha waja ambao amsendelela Mulungu kwanjila ya zabihu zizijha ambazo makuhani adaendekela kuchocha chaka pambuyo pa chaka pambuyo pa chaka. 2Au vinginevyo zabihu zimene sizidakukoza kukoma kuchochedwa? Kwa chigezo chimenecho amgwadia akakala achukidwa mara kamoji siadakala ndi utambuzi kupunda wa machimo. 3Nampho katika zabihu izi kuli nikukumbukila wamachimo yayoyadchitidwa chaka pambuyo pa chaka. 4Pakuti siikozekana kwa mwazi wa ojiwika ndi mbuzi uzichocha machimo.5Nyengo Kristo yapowadajha pajhiko, wadakamba, "siwadamkumbile machochedwe ya zabihu. Pambuyo pake, wadaandaa thupi kwachifuko changa. 6Simdali ndi mate katika machochedwe yonche ya kukwaniza au zabihu kwa chifuko cha machimo. 7Pothela wadakamba, "penya yapa niyachita mapenzi yako Mulungu, ngati umoyalembedwa kunihusu ine katika gombo"8Wadakamba ngati umoidakambidwa pamene pamwamba,"simdakumbile zabihu, machochedwe , au mphaso ya kutekelezdwa kwa chifuko chamachimo, wala siwadaone chisangalalo mkati mwake." Zabihu ambazo zichochedwa kulingana ndi lamulo. 9Pothela wadakamba penya, nilipano kuchita mapenzi chako." Waikapamphepete taratibu zilizoyamba ili kuimarisha zijha zakawili. 10Katika taratibu za kawili, thatotengedwa kwa Mulungu kwa chikondi chake kupitila kujichocha kwa tuphi la Yesu Kristo mara kamojhi kwa nthawi zonche.11Ni uzene kila kuhani kuima kwa huduma sikukuu a siku, niwachocha zabihu iijha, ambayo kwa valivonche kamwe siidakakozeka kuzichocha machimo. 12Nampho pambuyo pa Kristo kuchocha zabihu mara kamoji kwa machimo muyaya yonche, wadakala jhanjala lakuchimuna la Mulungu. 13Niwalindilila mpaka maadui zake ailidwe panchi ndi kuchitidwa mpando kwachifuko cha myendo yake. 14Pakuti kwanjila ya chochedwe limoji wakwaniza muyaya waja ambao atengedwa kwa Mulungu.15Ndi Mzimu Oyela nao ushudia kwathu, pakuti poyamba wadakamba. 16Ili ni lailano ilisinichite pamoji nao pambuyo pa siku izo, wakamba ambuye siniike lamulo langa mkati mwa mitima yao, ndi sinizilembe katika njelu zao.17Potela wadakamba, "siazindikilancho machimo ndi vindu vao mafu." 18Chipano pamalo palipo ndi kulekelela kwa anyiyawo pa libencho zabihu yaliyonche kwachifuko cha machimo.19Kwachimwecho, abale tilinao ujasili wakulowa pamalo poyela kupunda kwa mwazi wa Yesu. 20Chimwecho ni njila ambayo waichakula kwa chifuko chathu kwa njila ya mtuphi mwake, mpya ni umoyo iyoipitila papazia. 21Ndi kwa chifuko thilinayo ya kuhani wamkulu pamwamba pa nyumba ya Mulungu. 22Ni timsendelele ndi mtima wa uzene katika kukamilika wa uzenezene wa chitukuko tikakala ni mitia iyoyatilidwa safu kuchokela koipha kwaganizo ndi kukhala ndi mathuphi yathu iyoyachukidwa kwa maji ya bwino.23Basi ndi tigwililile kwa usabiti katika lailano la ujasili wa chikhuluphi chathu, bila yakung'anamuka, kwachifuko Mulungu wadahaidi ni oamika. 24Ndi tizidi kuganizila njila yakumtila mtima kila mmoji kukonda vinthu vabwino. 25Ndi tisidasia kusonkhanika pamoji ngati umoachitila winawake, kutilana mtima kila mmoji kupunda ndikupunda ngati umompenyela siku lilipafuphi.26Ngati tikachita vadala kuendelea kuchita machimo pambuyo pakukala talandila njelu ya zene, zabihu na yamachimo siikalilancho. 27Pambuyo pake, kulikukulupalila layokha lahukumu ya kuofya, ndi ukali wa moto apapo siwateketeze oipha Amulungu.28Walienche ambayo walikana lamulo la Musa kufabila rehema pachogolo pa ushuhuda awili au atatu. 29Kiwango chanji zaidi cha azabu uganizila chimfuna kila mmoji ambae wamdelela mwana wa Mulungu, walienche uyowaichita mwazi ya agano ngati nchinthu osati choyela , mwazi ambao udaikidwa wakfu kwa Mulungu waliyonche ambayo wamtukwana mzimu wa chimwemwe?30Pakuti tijiwa ambae wadakamba, "kiasi changa sinilipe," nditena, "ambuye siahukumu wanthu wake." 31Ni jambo la kuopecha munthu kugwela kupitil manja ya Mulungu wali wamoyo.32Nampho zindikila siku za mmbuyo, pambuyo pakutilidwa kwanu dangarila, ni jinsi yanji mdakhoza kuvumilia maumivu makali. 33Mdali mwaikidwa wazi katika zihaka ya malambwajho ndi mayeso, ndi mdali washiriki pamoji na anyiwajha adapitilila mayeso yaya. 34Pakuti mdali ndi mtima wa risungu kwa anyiyawa adali omangidwa ndi mdalandila kwa chisangalalo azabu ya osidwila wanu, nimjiwa kuti anyiimwe mwachinawene mdali ndi osidwila wabwino ndi wakulimba muyaya.35Kwachimwecho msidataya uasili wanu, uli ndi mphao yaikulu. 36Pakuti mfuna uvumilivu, ili kuti mpeze kulandila chilipo Mulungu wachihaidi, pambuyo pakukala mwato yachita mapenzi yake. 37Pakuti pambuyo pa kale kidogo, moji uyowakujha siwaje ndi hakika siwachedwa.38Mwene haki wanga siwalame kwa mtendele, ngati siwabwele kumbuyo sinimkondwela nayo. 39Nampho ife ngati wajha abwela kumbuyo kwa kugwa, pambuyo pake. Ife ni baadhi ya wajha tii ndi mtima ya kuzisunga mizimu yathu.

Chapter 11

1Chikulupi ndi uzene walinawo munthu pa vinthu ivo wavilindilila. Ndi uzene wa vinthu ivo vikali osaoneke. 2Pa ndande iyi achambuyatu adajiwika pa chikulupi chao. 3Pakulupalila tijiwa kuti jhiko lidalengedwa ndi lamulo la Mulungu. Kuti icho chidaonekana chidalengedwa kuchokela ndi vinthu ivo vidali vimaoneka.4Idali ndande ya chikulupi kuti habilu wadapeka kwa Mulungu chembe yooneka kuposa umo wadachitila Kaini. Idali ndande iye wadaelekedwa kuti wachilungamo. Mulungu wadamuelekela ndande ya mphoto izo wadapeleka, pandande iyi, Habilu wakhali kukamba, ingakale wa mwalila.5Idali chikulupi kuti Enock wadatengeda kumwamba ndi siwadafe. Siwadaoneke, ndande Mulungu wadamtenga pakuti padakambidwa pakati paiye kuti wadamkondwecha Mulungu wakali osatengedwa kupita kumwamba. 6Popande chikulupi siungate kumkondwecha Mulungu, ndande yake wapita kwa Mulungu ifunika wakulupilile kuti Mulungu walimoyo ndikuti apachidwa mphoto anyiwaja amchata.7Idali mchikulupi kuti Nuhu wadachenjezedwa ndi Mulungu pakati pa vinthu ivo vidali vosaoneke, mwa ulemu wa Chimlungu wadakonja chombo chifukwa cho ombolela wana wake pokachita izi wadalilamula jhiko lapanchi ndi kulandila chilungamo kujela chiulupi.8Idali Mchikulupi kuti, Ibrahimu yapo wadatandwa wadalemekeza ndikupita pamalo yapo wadafunika kulandila chilungamo. Wadachoka posajiwa kuti wapita kuti. 9Idali chikulupi kuti wakale moyo mjhiko ilo wa dalonjezedwaa ngati mlendo. Wadakala mmahema pamoji ndi Isaka ndi Yakobo, achilungamo anjake alonjezo la Mulungu. 10Pakuti wadafunika kupeza muji uo wadauganiza ndi woumanga wakadakala Mulungu.11Izi zidali mchikulupi kuti Abrahamu, ndi sara mwene, adalandila mphamvu za kutenga pathupi ingakale adali mikota kupunda, ndande adaona Mulungu ndi okulupilika, uyo wadaalonjeza mwana wa mmuna. 12Kwaicho kuchokela kwa munthu mmoji uyo wadali patupi kumwalila adabadwa wana osawelengeka, adaali ambili ngati nyenyezi za kumwamba ndi ambili ngati mchenga wa pagombe la nyanja.13Anyiywa onche adamwalia mkati mwachikulupi popande kulandia lonjezo. Ikapanda adaona kwa patali ndi kukondwelela. Adavomela kuti adali alendo ndi opita panchi pano. 14Anyiwaja akamba vithu ngati ivi aika poyela kuti afunafuna jhiko lao achinawene.15akhadakala kuti aganizira jhiko ilo adachoka, akadakala ndi malo yobwelela. 16Nampho ngati umo ili, akubila jhiko lilibwino ilo la kumwamba, kwaicho Mulungu siwaona manyazi kutanidwa Mulunu wao, pakuti wakonja mujhi ndande ya anyaiwo.17Idali ndi chikulupi kuti Ibrahimu pambuyo pakuyesedwa, wadamchocha Isaka. Etu, uyo wadalandila lonjezo mwachimwemwe, wadamchocha mwana wake yokha. 18Pa iyeyo padanenedwa, kuchokela kwa Isaka vibadwa vako sivitanidwe. 19Ibrahimu wadajiwa kuti Mulungu wadali ndi mphavu youcha munthu kuchokela kwa akufa ndi kunena pa mkmbo wa fanizo wadamlandila.20Idali mchikulupi kuti Isaka wadaaphemphera wana wake Yakobo ndi Esao pa vinthu va mchogolo. 21Idali ndi chikhulupi yapo wadamwalila Yakobo, waaphemphera wana wonche Ayusufu Yakobo wadatamanda ndikuyazamira pandodo yake. 22Idali ndi chikhulupi kuti Musa, yapowadabadwa wadabisidwa pa myezi itatu ndi makolo wake ndande adamuona kuti ndi mwana wa kanda uyo wadali wabwino, ndi sadaope lamulo la mfumu.23Idali ndi chikulupi kuti Musa yapowadabadwa wadabisidwa pa myezi itatu ndi makolo wake ndande adamuona kuti ndi mwana wa kanda uyo wadali wabwino, ndi sadaope lamulo la mfumu. 24Idali ndi chikulupi kuti Musa wali wamulu wadakana kutanidwa chijuku cha Farao. 25Pambuyo pake wadvomela kuzunjidwa pamoji ndi wana Amlungu pambuyo po sangalila machimo pa nthawi yaityali. 26Wadaganiza kuti manyazi ya kumchata Kristo kuti ndi ulemelelo waukulu kuposa mphoto za Kumisiripakuti wadagaza maso yake ku mphoto panyengo ya mchogolo.27Idali ndi chikulupi kuti Musa wadachokela Kumisiri, siwadaope mphwayi ya mfumu, pakuti wadalmba mtima pa kupenya kwa uyosiwaoneka. 28Idali ndi chikulupi kuti wadagwila chikondwelelo cha Paaka ndi kunyinyizila mwazi kuti owananga wa mbadwa oyamba wasakoza kwa agunda obadwa ayamba wachimuna Akuisraeli.29Pokhala ndi chikulupi kuti adapitila nyanja ya Shamu ngati pa mtunda, nyengo Amisiri yapo adayesa kudusa adamizidwa. 30Pokhala ndi chikulupililo kuti phupa la Kuyeriko lidagwa panchi, pambuyo pokazungulila masiku ya sano ndi yawili. 31Pokhala ndi chikulupi kuti Rahabu yuja mazi wa za dama siwadafe pamoji ndi anyiwaja adali asavele, chifukwa wadaalandil azondi ndi kuasunga bwino.32Ndi kambe chiyani kupunda? Pakuti nyengo sikwana kukambilila za Gidione, Barak, Samsoni, Yeftha, DAudi, Samweli ndi za aneneri. 33Yawo kujela chikulupi adagwecha maufumu adachita chilungamo, ndi adalandila lonjezo, adachekeleza chakumwa mikago. 34Adatimicha ukhali wa moto, ndi adapulumuka di mphamvu ya chikwanje, adapulumuchidwa ndi matenda, adali ngwazi kunkhondo ndi adatangicha magulu ya chilendo.35Wachikazi adawalandila wanthu wao yawo adamwalila a kwa ukicha, wina adazunjidwa popande kuvomela kuleleledwa kuti akhoze kuzowelela kuukicha bwino kupunda. 36Anjake adazunjidwa ndi kuaseka ndi kuwamenya, naam ndi kuwamanga ndi kuwaponya mndende. 37Adaponyedwa miala, adadulidwa vipinjili. Adaphedwa ndi chikwanje, amaenda ndi chikwetu cha mbelele ndi chikwetu cha mbuzi adali amphawi amaendekela ndi kuzunjidwa ndi kuchitidwila voipa. 38(Ivo jhiko silidafunike kukhala navo) amangoyendayenda mphululu, mmaphili, mmapanga ndi mmaenje ya panchi.39Ingali wanthu wonche adavomeleka ndi Mulungu ndande ya chikulupi chao sadalandile icho wadaalonjeza. 40Mulungu wadachogola kitininkha chinthu chili cha bwino, kuti popande ife sadaka khoza.

Chapter 12

1Kwaicho pakuti tazungulilidwa ndi mtambo okulu wa amboni ndi titaye kila chinthu icho chitimeleta pamojhi ndi machimo yayo yatipeza kwa sanga titamange liwilo kwa kulindilila mwa mpikisano yaikidwa pachogolo patu. 2Tipenye maso yatu kwa Yesu, wali oyambicha ndi mwene kumaliziha chikulupi chatu icho kwachifuko cha chimwemwe chaikidwa pachogolo pake wadalimbichila mtanda, wadaipepula nchoni yake, ndi kukala panchi jhanja la kwene wa mpando olemekezeka wa Mulungu. 3Mate muganizila iye wadalimbicha mau ya kuipilana kuchoka kwa uyo wali ndi machimo kupita iye mwene wake kuti msadajha kulema kapena kukomoka mitima yanu.4Simdavutike kapena kuyambana ndikupikisana ndim machimo mochepekela kutedwa mwazi. 5Tena mwayawalila kujhakutilidwa mtima uko kukutandauzilani ngati wana wa chimuna; "mwana wanga usadayatenga kwa mapepuka mabwelelo ya ambuye, wala usadakubwelela mbuyo yapo ukonjedwa ndi iye." 6Pakuti ambuye wampacha ulemu uyo wamkonda, ndi kumlanga waliyonche mwana uyo wamlandila.7Limbicha mayeso ngati kubweledwela. Mulungu wakonjekela ndi anyiimwe ngati uo wakonjekela ndi wana, ate ndi mwana yuti uyo atate wake siwakoza kumbwelela. 8Nampho ngati palibe kulamulidwa uko tawonche tidali kutumikila basi anyiimwe ndi osafunike ndi osati wana wake.9Kupitilila yonche, tidali di acha atate watu ajhiko wa kutibwela ndi tidalemekeza. Bwanji sitifunika ata kupunda kumvecha atate wa chizimu ndi kulama? 10Chazene acha atate watu adatilamula kwa vyaka vochepa ngati umoidaonekana sawa kwa anyiiwo, nampho Mulungu watilamula lawe faida yatu kuti titumikiie kuyela kwake. 11Palibe chihapilo chikondwelecha kwa nyengo imeneyo, chikala ndi kupyeteka. Ingakale chimwecho pambuyo pake chibadwa chipacho cha mtendele ukalo wa bwino kwa anyiiwo ayaluzidwa nayo.12Kwaicho kwezani manja yanu yayoyalenda ndi kuchicha maombono yanu yayoyahi opande mbhavu ikale iyo yali ni mbhavu ncho; 13Ongolani mopita mapazi yanu kuti yaliyenche wali opunduka siwachogozedwa motaike nampho siwapeze kulamichidwa.14Funani mtendele ndi wandhu wonche ndi mwemo kuyela ukopopande kumeneko palijhe siwakamwone ambuye. 15Mkale ojhipenyelela kuti wasadakalapo uyosiwapatulidwe kutali ndi lisugu la Mulungu ndi kuti usajha mtengo olujhukea uwosi upukile ndi kuyambukia mavuto ndi kuwananga ambili. 16Penyani kuti palibe chiwelewele kapena mundhu osamlemekeza Mulungu ngati Esau, uyo kwandande ya chakudya hiojhi wadagulicha malinga yake ya kubadwa. 17Pakuti mujhiwa kuti pambuyo yapowadakumbila kuganidwila mwawi wadakanidwa, kwa ndane siwadapate nengo ya kulapa pamojhi ndi atate wake pamojhi ndi kufuna kupunda kwa misozi.18Pakuti simdajjhe mwa pili ilo ukoza kugusidwa. Pili likelela moto mdima, kudelelecha ndi mafunde. 19Simdajhe kwa mkuwo wa mbetete kapena kwa mau yachokana ndi mkwo iyo idachiticha anyiayo amavela asadapempha mau lalilonje hunenedwa kwa anyiiwo. 20Pakuti siadakoze kuvumilia chijha chidalamulidwa; "ikakala ngati chiweto chagusa pili, nditu atimbiwe kwa myala." 21Cho ofya kupunda adachiona Musa wadanena, "naopa kupunda kufikilana kutentemela."22Pambuyo pake, mwajha mpili Sayuni mwa mujhi wa Mulungu wali wa moyo, Yerusalemu ya kumwamba, ndi kwa angelo elfu kumi anyiiyawo akondwa. 23Mwajha pa songhano la obadwa oyamba wonche alembedwa kumwamba, kwa Mulungu olamula wa wonche, ndi kwa mizimu ya oyela yawo ayenelechedwa. 24Mwajha kwa Yesu akonjechana wa mavomelezano ya chipano, ndi kwa mwazi uwo udamwaidwa uwo unena ya bwino kupunda mupitilila mwazi wa Habili.25Penyani kuti usadajha kumkana mmojhi uyo wanena. Pakuti ngati siadasendele yapoadamkana mmojhi uyo, watiyaluza pajhiko zene sitilama ikakala iting'anamukile kwa kutali kuchoka kwa yujha watiyaluza kuchoke kumwamba. 26Kwa nyengo imeneyo mkuwo wake udatingiza jhiko. Nampho chipano wachitila umboni ndi kunena, "ikala mara yenancho sinitingiza jhika loka, ikapanda kumwamba nako."27Mau yaya, "mara kamojhi ncho," ilangiza kuchochedwa kwa vindhu vijha ivo vapangidwa, kuti vijha vindhu vidatentemechedwe vikalile. 28Kwa icho, tilandile ufumu uwo siutentemechedwe, tikondwe mwa mtundu wa kumlambila Mulungu kwa kuvomela pamojhi ndi kujihichicha mwa kukundwelecha. 29Kwa mate Mulungu watu ndi moto ukudya.

Chapter 13

1Basi chikondi cha abale chiendekele. 2Msayawala kwa karibishe alendo, pakuti kwa kuchita chimwechi, wina wakaribishe angelo bila kujiwa.3Kumbukila onche ali mndende, ngati kuti mdali nao kuja pamoji nao, ni ngati matupi yanu yadachitida ila ngati anyiio. 4Basi ukwati ulemekezedwe ni wanthu onche ni basi chitanda cha ukwati chichitidwe kukala bwino, kwa chifuko Mulungu walamule amalaya ni achigololo.5Basi njila zanu za maisha zikale wazi katika chikondi cha ndalama. Mukale olizika ni vinthu muli navo, pakuti Mulungu mwene wadakamba, "simkusiani anyiimwe kabisa, wala kutelekezani anyiimwe." 6Basi tilizike dala tinene chichimi, "Atate ni otangatila wanga, simopa. Muthu wakoze kumchita chiani?"7Aganizileni aniwaja akuchogozani, anyiwaja akuchogozani, anyiwaja ali kamba mau la Mulungu kwanu, ni kumbukilani matokeo ya vichito vao! Esani chikulupi chao. 8Mpulumusi ni iye julo, lelo, ni ata muyaya.9Usafika kuchogozedwa ni mayaluzo yosiana siana ya chilendo kwan ni bwino kuti mtima umangidwe kwa mwawi, ni osati kwa lamulokuhusu chakuja yameneyo sijatangatila anyiyao akala kwa yameneyo. 10Tilinayo ambayo anyiyao atumika mkati mwa nyumba ya mapemphelo alije haki ya kuja. 11Pakuti myazi ya wanyamo, zidachochedwa sadaka kwa chifuko chi chimo, idapededwa ni wakulu anchembe mkati mwa malo yoela, nampho matupi yao yadabuchidwa kubwalo kwa kambi.12Kwa icho Mpulumusi nae wadazunjidwa kubwalo kwa kome la muji, dala kuti kuika sadaka wanthu kwa Mulungu kupitila mwazi wake. 13Ni Kwa icho tieni kwake kubwalo kwa kambi, tikatenga manyazi yake. 14Chifuko tilije pokala paodumu katika muji uno, badala yake tifune muji uo ukuja.15Kupitila Mpulumusi ifunika tetete kujichocho sadaka ya kumpempha Mulungu, kumwimbila kwa tunda la milomo yatu likili jina lake. 16Ni usayawala kuchita yabwino ni kutangatana anyiimwe, pakuti ni wa sadaka ngati imeneyo nde ujo Mulungu wakadilichidwa viwi. 17Lemekezani ni kujichicha kwa akuchogozani wanu, chifuko aendekela kulindani kwa chifuko cha mitima yangu ngati anyiwaja sachoche ivo achita. Lemekezeni dala kuti akuchogozani wanu akoze kukupenyelelani kwa chisngalalo ni osati kwa kudandaula ambako sikutangatilani.18Tupempheni chifuko tili ni uzene kuti lili ni chichimi cha bwino, tikumbila kukala maisha ya ulemu katika mambo yonche. 19Ni mwaonche mphavu za mbili mchite chimwchi dala kuti nikoze kubwela kwanu pafupi yapa.20Chapano Mlungu wa mtendele ambae wakupelekani kuchoka kwa akufaowesa mbelele wa mkulu Ambuye Mpulumusi kwa mwazi wa vomelwzano la muyaya. 21Wakupacheni kukoza kwa kila chinthu cha bwino kuchita funidwe lake, mwachita nchito mkati mwatu ili ya bwino niyokadwilicha pamaso pakekupitila Mpulumusi, kwa iye ukale ufulu Muyaya ni muyaya. Amina23Chapano nikutila mtima m'bale kutengelana ni mau la kutila mtima ambalo kwa chifupi mdalilemba kwanu. 22Mjiwe kuti m'bale watu Timotheo wasiililidwe uhru, ambae pamoji ni iye nikupenyeni ngati siwaje pafupi yapa.24Lonjela ochogoza wako onche ni okulupalila onche. Anyiwaja achoka kuitalia akulonjela. 25Ni mwawi ukali namwe mwaonche.

James

Chapter 1

1Yakobo, mtumiki wa Mulungu ndi ambuye watu Yesu Kristo, pa malamula kumi ndi yawili yayo yadakgawanyika, msalaam. 2Walengani kuti ndimtendele kupunda, bale wanga, yapompita pamavuto yasina siyana, 3mkaja ndi kuesedwa pa maeso yanu yakupachani kulimba.4Siyani kulimba tilimbiche njito yake, kuti mukoze kukwima kolimbika, bila kupunguzidwa palalilonje. 5Nambo ngati kuli mundu pakati patu uyo wafuna ulemu, wapembe kuchoka kwa Mulungu yao achocha ndiulemu ndi popande kukambicha ndi wonje wapemba, ndi siwanikge ulemu.6Nambo pemba pa ulemu, posakule ndi kuopa ningati mafunde pa nyanja, utengedwa ndi mbepo ndi kutuidwa kuno ndi uko. 7Pamboni uzene mundu uyu wasadakganizila kuti siwalandilidwe pembo lake kuchoka kwambuye. 8Mundunuyu wali ndi vifuko viwilin isati volimba panjila zake zonje.9Abale olumala afunika wajivune ndi kuima kwake pamwamba, 10ndawi iino m'bale olemela pakujichicha kwake, pandande siwachoka ngati duwa la mkonde pakuti pamunda ilowapita. 11Juwa lichoka ndi funda ndi kupyeleza ndukuumicha mitengo, ndi maduwa kugwa ndi ubwino wake ndikuopa mchumwecho wandu olemela ochafuka pakatikati pa njito yao.12Wabalikizidwa mundu yuja walimba pa mavuto, pakutu pambuyo kukoza uesedwa ili, siwalandile mboto ndikula, iyo yalembedwa pawaja akonda Mulungu. 13Mundu walionje wafunika kukumba yapo waesedwa, "esedwe ili lichoka ndi Mulingu," pa ndane Mulungu siwaesedwa ndi machimo, ndi Mulungu mwene siwamuesa walionje.14Kila mundu waesedwa ndijanje zake zoipa izo zimnyenga ndi kumkguza patali. 15Basi badala yajanje yachimo kubala mimba, chimo libadwa, ndi pambuyo pa chimo kukwima sawasawa, ndikuta panyifa. 16Abale wanga akondedwa, msadanyengeka.17Kila mboto ni iliyabwino ndi mboto yakamilika ichochichoka kumwamba, kunchika panji kuchoka kwa atate owara. Ndipo siwabaitika ngati mtunji usindao. 18Mulungu wadasanga kupeza ife kulama kwa mau lauzene pakuti tikoze kukala ngati ubado oyamba mmalo mwa vindu vake.19Mujiwa ili am'bale wnga okondedwa kila mmoji wafunika kukala upepuka ovela isati opepuka kokamba ndi kukwiya. 20Pakuti mkwiyo wa mundu siukoza kuchita uzene wa Mulungu. 21Pa ndande imeneyo ikani patali uchafu wa chimo ndi kuipa konje uli pamalo paliponje ndi pakujiopecha lilandileni mau lavyalidwa mkuti mwatu, ilo lili ndi mbavu ya kujiokowa mitima yatu.22Lilemekezeni mau msidalivela pe, msadajinyenga mitima yanu mawene. 23Pakuti ngati walionje alivela mau mau bila kuchita njito ndi sawa ndi mvundu wajipenyae pamaso pake pazene pa chiyo. 24Uvomelezeka pamaso pake ndi kupita zake ndi pambuyo pandawi yaifupi uiwala ivo wachita. 25Ndipo munthu yuja uyowapenya kojipenyelela lamulo lo jisiya ndi kwendekela kulemekeza, opande pandande iye ndeovevela uyo waiwala, uyu mundu siwabalikiwe yaposiwachite.26ikakala mundu walionje siwafike mwene kukala mundu wa dini nambo siwkoza kuuenela lilime lake, unyenga mtima wake ndi dini yake ndicha je. 27Dini ili bwino ndiiyo siwanangindwa pachogolo Pamulungu wandu ndatate ndi ili kwatangata wana alibe baba ndi mama ndi yao akuja poteseka pao, ndi kuwapenyelela yao ali niungurigu wa jiko.

Chapter 2

1Abale wanga msachata cha ambuye Yesu Kristo, ambuye oyela ko kondolela wanthu ochepa. 2Ngati munthu wa kuti wakalowa mmisonkhano yanu wavala mphete ya golide ndi nchalu zabwino kenaka wakalowa osauka wavala nchaluza kuda. 3Ndi mkalangiza kumsamala yuja wa nchalu za bwino ndi kukamba "chonde iwe kala ya pamalo pabwino" nampho mkamkambile yuja osauka "iwe ima yapo" kapena kala panchi yaa myendo yanga. 4Bwa simlangana mwachina wene, ndi kukala olamula maganizo yoipa?5Vechelani abale wanga okondedwa, Bwa Mulungu siwada asankhule asauka ajiko kukala olemela mu chikulupi ndi kusiidwila ufumu wa pangano kwa okondedwa? 6Nampho mwapepula osauka Bwa osadi ole melawa akuvutani anyiimwe, nd anjiiwo akuguzani mmalamulo? 7Bwa opande olemelawa alitukwana jina lija la bwino lene amjiimwe mwatanidwila.8Ingakale ngati mwakaniliza lija tauko la chifumu ngati umo yalembedwa mmalembo, siumkonde wapafupi ngati umo ujikondele wamwene muchita bwino. 9Nampho ngati mukondelela wanthu akumoji mchita machimo, mlangidwa ndi tauko kukala otyola tauko.10Ndande walionche wavomela matauko yonche ndi wakali, wakajikuwala wakala ndi mlandu otyo la matauko yonche. 11Ndande Mulungu wadakamba usadapa, ngati siuchita chigololo nampho ukupa, watotyola tauko la Mulungu.12Kwa icho kambilanani ndi kuvomela ngati yao muli pafupi kulangidwa ndi tauko la ufuru. 13Ndande chilango chikuja popande lisungu kwa yao alije lisungu, lisungu likwela pamwamba cha chilango.14Kuli kukwada kwanji, abale wanga, ngati munthu wakamba ndili ndi chikulupi, nampho walibe vichito? Chikulupicho chikoza kumpulumucha. 15Ngati m'bale wammuna kapena wamkazi wali ofuna nchalu kapena chakudya cha kila sku. 16Ndi mmoji wanu wakaambalila mapitani mwamtendele, mkaote moto ndi mdye bwino nampho simwapacha chofuna cha tupi imehe itangatila chiyani? 17Ingakale chikulupi choka popande vichito chafa.18Ikali munthu wa kuti wakoza kuamba uli ndi chikulupi, ine nili ndi vichito, nilangize chikulupi chako popande vichito, nane sinikulangize chikulupi changa ndi vichito. 19Iwe ukulupilila kuli Mulungu mmoji, ulibwno nampho mizimu ikulupilila chimwecho ndi kutethemela. 20Bwa ufuna kujiwa iwe munthu opande malango umo chili chikulupi chopande vichito chosatangatile?21Bwa osati atate watu Abraham adawelengedwa malinga kwa vichito yapo adamchocha mwana wao Isaka pamwmba pa madhabao. 22Muona kuti chikulupi chake chidachita nchito ni vichito vake ndi kwa vichito vake chikulupi chake chidafikila dala lake. 23Malembo yadakwanilichidwa yaya yakamba "Abraham wadamkulupilila Mulungu ndiku welengedwa wa malinga" kwa icho Abraham wadatanidwa mbwenji wa Mulungu. 24Muona kuti kwa vichito munthu wawelengedi wa malinga osati kwa chikulupipe.25Ingakale Bwa osati Rahabu yupa wa chigololo wadawelengedwa malinga kwa vichito yapo wadalandila apungwe ndi kuapeleka kwa njila ina? 26Ndande ngati umo ili tupi popande mzimu lafa ingakale chikulupi papande vichito chafa.

Chapter 3

1Abale wanga, osati ambili wanu mfunika kukala mpuzusu mkajiwa kuti sitilandile lamulo lalikulu kupunda. 2Pakuti taonche tilakwila kupila njia za mbili, ngati walienche kapena siwajikonda kupitila mau yake, mmeneyo ndi muntu okamilika wakoza kulichekeleza tupi lake lonche mwene.3Chopano ngati tiika vochuchuluka mkati mwa mkamwa mwaameneo ativemeleza ndikoza kung'anamula matupi yao yonche. 4Jiwa kuti meli, atangati yaikulu ila isukumidwa ndi mphepo yokalipa, zichogozedwa ndi msukano waung'ono wana kupita paliponche uko achokela anahodha.5Chimwechija, lilime ndi chiwalo chaching'ono cha mtupi, nampho kujienelela madama sana mpenye pululu lalikulu umo likozela kubuchika ndi cheche ya ing'ono ya ing'ono ya moto. 6Lilime nalo ndi moto, ndijiko lolakwa, waikidwa mkati mwa viwalo vamtupi mwao, kapena uchafu mtupi lonche ndikuika kumwamba ndi moto njila ndi maisha ya achinawene kubuchidwa ndimoto wa kuzimu.7Kila mtundu wa chinyama chamtengo, mbalame ndiichochikwawa ndi chiumbe cha mnyanja chichekelezedwa ndi wantu. 8Nampho polibe muntu hata mmoji uyowakoza kuchekeleza lilime, ndikulakwa uo sidatulie, wajala sumu yabisika.9Kwalilime ndikulemekeza ambuye ndi baba untu, ndi kwa mmeneyo twawalani wantu oumbidwa mfano wa Mulungu. 10Kuchoka mkamwa mwake kukambamau ya bwino ndi yoleswa. Abale wanga vintu vinosivifunika.11Bwa, chitume chimoji yookoma ndi yowawa. 12Abale wanga, Bwa mtengo wa mitengo ukoza kubala vipacho va mizeituni, kapena mzabibu ubala vipacho va mumtengo? Osati chemchemi maji.13Yaani mmneyo walimkati mwanu walindulemu ndi kujijiwa. 14Nampho ngati mulikuipidwa kopitilila ndi maganizo ya weka mutima mwanu simdajiganizi la ndikukamba mtila ndi muukana uzene.15Uo osati ulemu uja uchitika kuchoka kumwamba nampho pambuyo pake ndi wajiko osati ya mtima ndi ya mzimu. 17Pakuti pamepo pali mtima oipa ndikujifunilaweka palipo kuli posa gwilizane paliponche pali vichito voipa. 16Nampho kujichicha kuchokel kumwamba poyambila ndi pabwino. Pambuyo pake kukonda mtendele kudeka ndikwakufunila wena ya bwino yalikuja kulekelela ndi vipacho va bwino popande kuimila kumoji ndi uzene. 18Ndi chipano cha uzene chivyalidwa pamtendele kwa achaneo achita ya uzene.

Chapter 4

1Ndeo ndi kuyambana mkati kati mwanu vichoka kuti? Siviime kuchika pa nchanje zanu zoipa zipeleka ndeo mkati mwa umoji wanu. 2Mkumbila chija mlije. Mkupa ndi kujifuna chija kumkoza kukala nacho. Mbulana ndi kuyambana ndi mkali simpata kwa ndande simumphompho Mulungu. 3Mphempho ndi simlandila kwa ndande mpempho kwe vinthu voipa kuti mkoze kuvitumikila kwa kumbilo lanu loipa.4Anyiimwe achigololo simjine kuti ubwenji ndi jino ndi kuipichana ndi Mulungu? Chapano waliyonchhe walamula kuti bwenji wa jiko wajichita oipa kwa Mulungu. 5Kapeno mganiza malembo yalibe mate yakamba kuti mzimu wauika mkati mwatu wali ndi nchhanje yaikulu kwa ndande yatu?6Nampho Mulungu wachocha lisungu la likulu ndo ndande malembo yakamba, "Mulungu wamkanila wali ndi mbwinya, nampho wampacha mwawi ojichicha". 7Kwa icho jichocheni kwa Mulungu. Mkaneni sata na ndiiye watawe kuchoka kwanu.8Sendelelani patupi ndi Mulungu, ndiiye siwasendelele patupi ndi anyiimwe. Kadwilichani manja yanu, anyiimwe olakwe, ndi mjichuke mitima yanu anyiimwe muli ndi maganizo yawili. 9Dandaulani, ganizilani ndi kulila, ng'ona muloni chiseko chanu kukala dandaulo la kukondwa kwanu kukale maganizo. 10Jichicheni mwachina wene pauchogolo pa ambuye, ndi siwakunyakuleni kumwamba.11Msakambilane voipa anyiimwe kwa anyiimwe, achabale. Munthu onene voipa ndi mbale wake ndi kumlanga mbale wake, kunena ndi tauko ndi kuilanga tauko la Mulungu. Mkalanga tauko, simuitemekeze tauko mlilanga. 12Ndi mmoji pe wali mchoche tauko ndi kulamula, Mlungu, iye wali ndi mphavu zo lamicha ndi kupa. we ndi yni umlonga wa patupi wako?13Vechelani anyiimwe mkamba, "lelo kapena mawa tipite katika muji uundikukala chaka kumeneko ndikuchita malonda, ndikukonja pandu. 14Ndi yani siwajiwe chiyani chichikele mawa, ndi lamidwe lamu ndi chiani? Pakuti mlingana ngati pundulu o uchokela kwa nthawi yaifupi ndi kusowa.15Pambuyo pake mdakakomba, ngati chifuno cha mbuye tilame ndi sitichile rehi kapoa roho. 16Nampho sino mjielekela chifuko cha vochitavanu doma vonchela ndi volakwe. 17Kwa iye wajiwa kuchita vabwino nampho namphosiwavichita kwaiye ndi kulakwa.

Chapter 5

1Majani chipana, anyiimwe mulindi ulemelela, lilani kwa sauti ya pa mwamba ndande ya taabu iyoikuja pamwamba panu. 2Ulemelela wanu wawangidwa ndi nchalu zanu zatafunidwa ndi viduduva wananga. 3Dhahabu zanu ndi ndalama zanu za kuso thamani ndi kuwananga kwake si si ushuhudie mkati mwanu ndi kupwetekedwamnthupi mwanu ngati moto. Mwajiikila akiba yanu kupitila siku zoonthela.4Penyani, malipo ya achita njhintha waja anyiao simdalipe ko vuna kupitila minda yanu atolila! Ndi chililo cha anyiwaja avuna mazao yanu cha fikila mmakutu ya ambuye amajeshi. 5Mwaishi kwa achima pajikha ndi kujilemekeza mwachinawene. Mwaji jumba licha mitima yanu kwa siku ya machinjo. 6Mwahukumu ndi kumpha mwene haki uyo siwakhoza kukukanilani.7Chipano vumilianani abale mpaka kuja kwao ambuye, ngati alima kulindilila vovuna vathamani kuchaka kupitila jikho , wakalindilila kwa kuvumilila ndande yake, mpaka vulazo yambila ndi zija zonchela zinyeche. 8Nampho anyiimwe mkhale ovumiliya mjigaze mitima yanu, ndande za kuja kwake Mbuye ndi kalibu.9Abale, msimanung'unikiana anyiimwe kwa anyiimwe, ili kuti msidaja kuhumidwa. Penya hakimu waima pa khamo. 10Kwa mfano, abale, penyani mateso kuvumiliya kwa olosa anyiyawo ada kamba kipitila jina la Ambuye. 11Penya, ntatana anyiwaja a vumiliya, "mbasa". Mwovela kuvumiliya kwa Ayubu, ndi mji wa dala la ambaye ndande ya Ayubu, ndande chiyani Ambuye ujata lisungu ndi kulekelela.12Zaidi ya yonche achabale wanga, simda lapa, au kwa kumwamba ama kwa pajikho, au kwa kiapo cha aina inancha. Chipano ebu "etu" yanu ndi imaanishe "etu" au "nantho" yanu ndi imaanishe "nantho" ili kuti msidaja kulowapachipo hukumidwa.13Pali wali yonche mkati mwanu wali ndi mavuntho lazima wapempho. Bwa, munthu waliyonche nde mwone kuchangamka? Ndi waimbe sifa. 14Bwa, kuli waliyonche mkati mwanu uyo wa dwala? Ndi watana midala akanisa, nao midala a kanisaapemphele pa mwamba pake, ajimpaka mafuta kupitila jina la Ambuye. 15Ndi mapemphelo za chikhulupalila siya mlamiche oduala, ndi Ambuye si amwimike ndi agati siwakhale wachita va chimo, Mulungu siwamlekelele.16Chipano muungame va chimo vanu anyiimwe kwa anyiimwe, ndi kupemphelana kila mmojindi machake ili mkoze kulamichidwa. Mapemphelo ya mwene haki kubala matokeo yayakulu. 17Eliya wadali munthu mene hisia ngati zanthu wadapempha kwa juhudi kuti vula inyenche ndi idanyencha pa jhiko kwa nyonga za vyaka vitatu ndi miezi sita. 18Ndi Eliya wadapempha, ndi kumwamba zidagwa vula pa mwamba pa jhiko ndi jikho yada chaka mavuno.19Acha bale wenga agati wodiyanche mkati mwanu wawanangika kuchoka kwa uzene nampho muthu mwina wambuozancho. 20Ebu wajiwa kuti waliyonche wachogoza mwine chima kuchoka katika njila yake ya la kwila si walamichidwe mtima wake kuchaka kamang.amung'amu ndi kuvinikilidwa vambili va chima.

1 Peter

Chapter 1

1Petro mtumiki wa Yesu Kristo, kwa alenda o sambazika, ka ochaguludwa, kupitila pantu yanche Galatia, Kapadokia, Asia ndi Bithinia, 2kuchakana ndi njelu ya Mulungu, tate, ko chukidwa ndi mtima ayela, kwa ulemu wa Yesu Kristo, ndi kwa nyunyuzi lidua mwazi wako. Neema ikhale kwanu ndi mtendele wanu uongezeke.3Mulungu tate wa ambuye wanthu Yesu Kristo ndi adalisidwe. Kupitilila ukulu wa rekelela lako, wadatiningha kubalidwa ka chapano ndi ujasiliwa kulisi kupitila kuuchi dwo kwa Yesu Kristo kuchako kwa akufa. 4Kwa urithi uwasiupwotekedwa, siukala ndi uchafu wa kupungua, waifadhidwa kumwamba kwaajili yanthu.. 5Kwa kukoza kwa Mulungu mlindikwa kipitila chikulupi kwa kuokoledwa anyiyawa ali tayari kuchakulidwa kupitila nyongo zao nthela.6Chisangalala kupitila ili, ningakhale sainoni lazima kwanu kujivela huzuni kupitila majalibu ya namna zambili zambili. 7Imeneya imeneya ndande ya chikulupalilo chanu chikaze kuesidwa, chikhulupalila ambacho ndi cha thamani kuliko dhhahabu, iyo itaika kupitila mata ambaouesa chikhulupalila chanu chapate kubala sifa, kutukuzidwa ndi ule mddo kupitila kuchakulidwa kwa Kristo Yesu.8Simda muone iye , lakini mumkonda. Simumuona chipano, lakini mumukhulupalila kupitila iye mulindi chisanga lalo icho sichi khoza kuelezedwa kwa chisangalala icho chajala ndi kutukuzidwa. 9Chipano mlandila mwachinawene matokeo ya chikhulupi chanu, kuokoledwa kwa mitima yanu. 10Olosa adafunafuna ndi khufuncha kwa uzene kuhusu kuokoledwa uku, kuhusu mwawiamba udakakha wanu.11Adafunafuna kujiwendi mtundu wanji wa kuokoledwa ambako kudakaja. Adafunafuna njha kujiwa ni nthawi yanji mtima wa Kristo wali mkati mwao wamakamba chiyani na anyiiwo ii ichakela kupitila yapo wamakambila mapema kuhusu mavuto ya Yesu Kristo ndi kuyola ambako kudaka mchanta. 12Idamasulidwa kwa orosa kuti orosa kuti adali amavichitola vinthu ivi ndi popande ndande yao achinawene,, nampho kwa ndandi yanu kukambilila kwa vinthu ivi kupitila waja yao apeleka maula Mulungu kwatu panjila ya mlima oyelauyowadatumidwa kuchaka kumwamba, vinthu ivi atangela akhumbila kumasulidwa kwake.13Chipana mangani viuna va njeru zanu. Mukhale otulia kupitila maganizo yanu. Mukhale ndi ujasili mkamilike kupitila mwawi ambao siupelekedwe kwanu nyenga ya kumasulidwa kwa Yesu Kristo. 14Ngati wana aulemu, simdamangidwa mwachi na wene ndi kumbilo ambalo mdalichota nyengo mdali palibe njeru.15Nampho ngati uno walioyel iye wakutanani namwe kalani oyela mvichita vanu muukhalo wanu. 16Pakuti yalembedwa "khalani oyela ndande nine nili oyela". 17Ni ngati mutana ambuye waja alanga kwa malinga mwa nchita ya kila munthu, tengani nthawi ya ulendo wanu majichicha.18Mujiwa kuti sidakhale pandalama au zahabu vinthu iva viwanangika ivo taokoledwa. 19Nampho mwaomboledwa ndi mwazi wa ulevu wa Kristo, ngati ya mbelele yapande ukadili.20Kristo wadasanghidwa likali asakanjedwe jhiko nampho chapao nthawi lino zotela, wamasulidwa kwanu. 21Mumkhulupalila amulungu kupitila iyo Mulungu wa damuucha kwa akufa, mmene Mulungu wadamnikha kuyola kuti chikulupi chanu ndi kujichacha kwanu kukale mwa Mulungu.22Mwachita mitima yanu kukala ya bwino kwa ulemu wa uja uzene, kwa ndande ya chikondi cha chibale chasapinde, kwa icho mkondane malimbikila kuchokela muutima. 23Mwabadwa kwa kawili, opande kwa mbeu iwanangika, nampho kuchokela mbeu iyo siiwanangika, kupitila umoyo ndi mau la Mulungu ilo lakhalila.24Pakuti matupi yonche ngati machamba ndi kuyela kwake kanche ni ngati dua la chamba chambandi kugwa. 25Nampho mau la ambuye likhalila nthawi zonche u ndi utenga udalaliidwa mu mau la Mulungu kwanu.

Chapter 2

1Kwa icho ikani pamphelepete volakwa vonchhe, kunamiza, nchhele, nchhanje ndi mwano. 2Ngati wana wang'onong'ono, mkumbila, mkaka wa bwino wa mzimu, kuti mkoze kukula mkati mwa ombolelo. 3Ngati mwalawa kuti ambuye ndi abwino.4Majani kwa iwa ali mwla uo ulama uwo wakamidwa ndi wanthu nampho ilo lasankhidwa ndi Mulungu ndi la male kwa iye. 5Anyiimwe namwe ngati nyalayili ya moyo yamangidwa kumwamba inate nyumba ya mzimu, dala kuti utumiki oyela uwo uchoeha nchhembe za Mzimu izo zivomeleka kwa Mulungu kupitila mpulumusi.6Lambo likamba chimwechi. Penyani, naika Kusayuni mwaka wa pamphepete waukulu ndi uwo wasankhidwa ndi la mate. Waliyonechhe wakulupalila katika iye siwaona nchhoni.7Kwa icho ulemu ndi wanu kwanu anyiimwe mkulupalila nampho". Mwala wakanidwa ndi omanga kuti lakala mwala wa ukulu wa pamphepete. 8Ndi "mwala ajikowala ndi chimwala" anyiio ajikwala, alikana mau kwa lija adasa nkhidwa nalo.9Nampho anyiimwe ndi kamu lasankulidwa uttumiki wa chifumu. Pajiko lo ela, wanthu openyelela amlungu kuti mkoze kulangaze vichito voda bwicha va ijuja wakutanani kuchoka kumdima kuja kumwanga wake odabwicha. 10Anyiimwe poyambila simdali wanthu, nampho saino anyiimwe ndi wanthu amlungu anyiimwe simdalandile kulekelaledwa, nampho saino mwalandila kulekeleledwa.11Okondedwa, nakutamani ngati atendo ndi obeluka beluka kujimona kuchoka kukumbilo loipa la volakwa. Ivo vibuloma ndeo ndi mizimu yanu. 12Ifunika kukala ndi vichilo vabwino pajiko, dala kuti ata akaliamba kuli mwachita vinthu volakwa, sazipenye nchhito zanu za bwino ndi kumtomonda Mulungu katika siku yobwela kwa iye.13Lemekeza malamulo ya munthu kwa chifuko cha ambuye ikakala ngati mfumu wa mkulu. 14Ikakala olamula atumidwa kulanga ochita voipa ndi kwaelekela ochita vabwino. 15Pakuti ndi chikondi cha Mulungu, kuti kwa kuchita vabwino mwakalicha chete nkhani zo pande mate za wanthu owewela. 16Ngati wanthu olekeleledwa msatumikile kulekeleledwa kwanu kuchekeleza voipa, ndipo mukale ngati atumiki Amulungu. 17Alemekezeni wanthu onchhe. Akondeni mabale, Muopeni Mulungu. Mlemekezeni yamu.18Atumiki lemekezani fumu zanu kwa ulemu onchhe, osati fumu ali abwino ndio jichicha nampho ata oipa. 19Pakutindi kuelekela ngati waliyonchhe siwaembekeze mbweteko nyengo ya mavuto popande haki ndande ya dhamiri ya Mulungu. 20Ndi pindu lanji ngati mkala kuchita chino potela mlongidwe? Nampho ngati mwachita vabwino nde yapo simvutike kolangidwa ndipo simuelekezedwe kwa Mulungu.21Kwa ichi mdatanidwa kwa ndande ya mpulumusi nampho wadavutichidwa ndande yanu, wakusiilani chilangizo ndande yanu kuchata mapazi yake. 22Iye siwadachite chimo, siwadaonekane wa unomi mkamwa mwake. 23Nyengo wadatukonidwa, siwadabwelezele matukano, yapo wadavutichidwa, siwada offe wadajichoche mwene wake kwa iye olamula kwa haki.24Iye mwenewake wadasenchhela machimo yatu mkati mwa tupi latu pamtengo kuti tisida kala malo ya chimo, ndikuti tikale kwa haki. Kwa kutimbidwa kubuke anyiimwe mwalame. 25Onche obelukabeluka ngati mbelele idasowa, nampho sazima mwabwela kwa owesa ndiopenyelela milima yanu.

Chapter 3

1Kwa njila iyi anyiimwe muli wa iye mfunika kuchocha kwa chamunamu wanu mwachi nanawene kuti ngati akumoji amene siadalilemekeze mau, kupitila ukalo wachakazao akoza kuguzidwa popande mau. 2Kwa ndande yawo achinawene siakale aliona akalo lanu la lokadwa pamoji ndi ulemu.3Iyi ichitike osati kwa madua ya kubwalo - kumanga chichi, vinthu va dhahabu, kapena vovala va mtundii. 4Nampho pambuyo pake ichitike mwa uchimunthu wa mkafi mwa mtima, ndi kupunda mwa ubwino mwa kujichicha ndi kupola kwa mtima ndicho cha mtengo pamaso pa Mulungu.5Pakuti wachikazi oyela adajikonjeleza achinawene kwa njila iyi. Wadali nndi chikulupi mwa Mulungu ndi adajichicha kwa achamunao achinawene. 6Kwa njila iyi Sara adajichicha mwa Ibrahimu ndi kumtana iye mamuna wake. Anyiimwe chipano ndi wanawake ngati simchite yayo yabwino ndi ngati si mwopa voipa.Kwa njila imweyo imweyo anyiimwe wachimuna mfunidwa kukala ndi achakazanu, nimzindikila kuti anyiiwo achanjanu wa chikazi uponde mbhavu. 8Chipano, anyimwe mwawonche mukale ndi nia imoji, walisungu, chikondi ngati abale, ojichichia ndi opola. 9Msabwezela choipa kwa choipa, kapena tukwano kwa tukwano. Pambuyo pake mwendekele kudumisa chifuko iyi mdatanidwa, kuti mhoze kulandila dariso.10Iye afuna kukonda kukala ndi kuliona sikuhabwino lazima wachekeleze lilime lake kwa yoyipa ndi milomo yake kumena yosafunike. 11Ndi wang'anamuke ndi kusia yoipa ndikuchita ya bwino. Afunefune ntendele ndi kuuchata. 12Maso ya ambuye yamwona uyo wahi wa malinga ndi makutu yake kuvela mapembhelo yake. Nampho mphumi ya ambuye ulichinyueme shianyiyawo achita voipa.13Ndi yani siwakuwanangeni anyiimwe, ngati mwakumbila ilo lili bwino? 14Nampho ngati mvutika mwa malinga muli ndi dariso. Msadaopa yaja anyiiwe ayaopa. Msadakala ndi mantha.15Pambuyo pake mumuike Kristo ambuye mwa mitima yanu ngati woyela. Kila nyengo mukale chonga kumuyagha kila munthu uyowakufunjhani anyiimwe ndanda chiyani mulindi chikulupi mwa Mulungu. Chitani chimwechi mochika ndi uhemu. 16Muhole ndi maganizo ya bwino kuti wantu atukwana kalo lanu la bwino mwa Kristo akole kujipeza alinijhoni chifuko ananena ya kumbuyo dhidi yanu ngati kuti mdali ochita voipa. 17Ndi bwino kupunda ngati Mulungu wakumbila kuti mvutika kwa kuchita vabwino kupunda kuchita voipa.18Kristo naye wadavutika mara kamoji chiuko cha machimo. Iye ndiye wafi ndi malinga wadavutika ndande yaife, ndipo tidali ndi malinga, idalikuti atipeleke ife kwa Mulungu. Wadata chitupi, nampho wadachitidwa wa umoyo chi zimu. 19Pa chizimu, atapita ndi kulalika mizimu iyo chipano zili mndende. 20Sizidali zojichicha nyengo chiyembekezo cha Mulungu yapo umalindila nyengo ya Nuhu. Siku za kukonja safina ndipo Mulungu adapulumucha wanthu wochepa - mizimu - nane - kuchoka mmayi.21Ichi ndi chizindikilo cha ubatizo uwo upulumucha anyiimwe chipano, osati ngati kuchuka ukadiri kuchoka mtupi nampho ngati pembo la kufuna ubwino kwa Mulungu, kupitila kuhyuka kwa Yesu Kristo. 22Iye wali kujanja la kwene la Mulungu. Wadapita kumwamba; angelo malamulo ndi mbhavu nditu vimlolele iye.

Chapter 4

1Pandande, pakuti Kristo wadateseka patupi, jalani zida zavindu vivija. Iye wadateseka patupi wachakana ndi chimo. 2Mundu uyu waendekelajo kulama panjanje zatupi, isati kokonda kwa Mulungu, ko lama kwake yayoyadakalila.3Pakuti ndawi iyowapitil yakwana kuchita vindu ivo wandu wena avifuna kuchuta ungungu, vindu voipa, kukojela, lujo, chisangalalo cha usasali ndimapembelo yachifanifani zili ndimisozi. 4Akuganizila ndi kudabwa yapowajikwepecha kuchita vindu ivo pamoji nao, pamenepo akamba voipa pamwamba panu. 5Sachoche chiwelengelo kwauyo wali tayali kulainga yao ali amoyo ndi afa. 6Pandande ili pembelo lidambilidwa kwanu yaoadate kufa, kuti ingakale adato lamulidwa patupi lao ngati wandu, ili akoze kulama ivo wafunila Mulungu patupi.7Mmatelo wavindu vonje ubwela, pandande, mkale ndikujiwa icho chili ndiuzene, ndichikale ndi janje yabwino pakuti pa vindu vanu. 8Pambuyo pavindu voje, kalani ndikujituma pachikondi ndi kila mmoji pakuti chikondi sichifuna kuvunukula machimoo ya wina. 9Langizani ulemu ndikila mmoji ndi popande kulaumu.10Ngati umoili kila mmoji wanu ivy owalandilila mbavu, muitumie po langa, ngati aimilila abwino a mbavu zambili izozachochedwa chaje ndi Mulungu. 11Ngati mundu wakakamba, ndi ikale ndi kulingana ndi Mulungu, ndi ngati mundu watumika, ndi iwe ngati mbavu wadaningidwa ndi Mulungu wapate kukuzidwa kupitila Yesu Kristo ufulu ndi kukoza vili ndiiye muyaya. Amina.12Okondedwa msidawalenga maeso yayo yakuja kukuesani ngati chindu cha chilendo, ngakale kuli chindu cha chilendo icho chima chitika kwanu. 13Nambo kwa umo mpundila kupeza chizo welezi cha kuteseka kwa Kristo, sangalalani, ndipo kutimseke ndi kuyangalila pa chivunukulo cha ufulu wake. 14Ngakale mutakanidwa panjila la jina la Kristo, wadalisidwa, pa ndande ya mzimu wa ufulu ndi ufulu wa Mulungu wakala pamwamba panu.15Nambo pasadala walionje watedwa ngati wakupa, mngungu, wachita voipa, au uyo wajituma ndi vindu va wino. 16Nambo ngakale mundu wateseka ngati Kristo, wasadaona njoni, bali wamuyamike Mulungu pajina limenelo.17Pakuti ndawi yafika ndi chilango kuyambila panyumba ya Mulungu ndi ngati iyamba kwatu, sikale bwanji kwa waja savomela mau la mnungu? 18Ndi ngati "mwene malinga wapulumuchidwa kupitila volimba, sikale bwanji pa muntu walibe malinga ndi wali ndi chimo?" 19Chocho afe ateseka kuchokana ndi chifuno chamulungu wapacha chikondi chao cha kulenga okulupilila ndipo ndiwachita vaubwino.

Chapter 5

1Ndikupempani okota mkati mwanu ine ndili okota mnjao ndi mboni wa masauchonya Kristo ndichimojimoji mkara pakati paufuru siukalepo. 2Kwaicho ndikupacheni mtima anyiimwe okota lisungeni guru la Mulungu lili mkati mwanu lipenyeleleni osati ndande mfunika nampo chifukwa mkumbila chimwecho kuchatana Ndimulungu. Lipenyeleleni osati kwa kukonda ndolama za manyazi nampo kwa kukonda chabe. 3Msaada jichita agalu pamwamba pawantu alipa kupenye leledwa kwanu. 4Pamene osunga wa mkuru siwa lengizidwe simulandile chisoti chaufuru wosataicha mateyake.5Chimojimoji anyiimwe anyamata wa ng'ono ji chicheni kwa wa akuru wanu onyiimwe mwaonche valani kujichicho ndi kutandizana mwa achinawene kwa mwaachinawene chifukwa Mulungu waakaniza wantu ambwinya nampo waapa chs mtendele ojichicha. 6Kwaicho jichicheni panchi pajanja la Mulungu lili ndi mpavu dala kuti akwezedwe kwa ntawi yake. 7Mwiikileni mavuto yanuyonche pa mwambapaiye chifukwa wa kutengelelani.8Mkale ndi kulemekeza, mkale ojipenyelela yuja mdani wanu satana ngati mkango walulumo ndikunyemelela ndiwa funafuna waku mvuluza. 9Muime posa mchatila iye mkale ndi mpavu pakati pa landi lo lanu ukundimujiwa kutiacha bale wenu ali mjiko aendela mavuso ngati yameneyo.10Pambuyo pamavuto ya ntawi ya ifupi Mulungu - wo kulupiika wadakuta nani pakati pa ufulu wosata mkati mwa Kristo siwakuchilikeni ndi kuku imililani ndi kuku pachani mpavu. 11Ufuru ukale kwaiye ntawi zonche kwa ntawi zonche.12Ndikana navo kuti siwalo ngati mbale osunga yabwino ndi n kulembelani anyaimwe mwa chidule kuchatila kwaiye. 13Ovemela ali ku Babeli asankulidwa pamoji ndianyiimwe akulonjelani ndi maiko mwana wanga wakulonjelani. 14Mlonjelane muntu ndi mnjake kwa kupwanyana machokaya ya chikondi ndimfendela ukale kwanu amene muli nkati mwa Yesu.

2 Peter

Chapter 1

1Simoni Petro, mtumiki wa mbuye Yesu Kristo, payao alandila chikulupi chija cha ulemu ngati umotalandilila ife, chikulupi chilimkati mwahaki ya mulungu ndi uombola wandu Yesu Kristo. 2Ulemu ukale pamtendele uongezeke kupitila malango ya Mulungu ndi mwana watu Yesu.3Kupitila malango ya Mulungu tapata vindu vake vonje pa ndande yamalamulo ya unkalo, choka kwa Mulungu watiitana panjila ya ubwino woyela wake. 4Panjila i adatumanishila hadi yaikulu ndi chantengo wadachita ichi pamofi ndi kudichita tikale asiidwila vindu va Mulungu, pachiuko choendekela kuya machimo jiko lino.5Pa ndande iyi chiani changu imonjeza ubino panjia ya chikulupi chatu pandande ya ubwino, wazelu. 6Kupitila zelu, ndikupitila pangono kudikila ndikupita kulinda kuyela. 7Kupitila kuyela chikondi cha m'bale ndi kupitila chikondi cha m'bale chikondi.8Ngati ivi vilimkazi mwatu, vikaendekela kukala muntima mwetu, pamenepo ife sitikula asabale pina wandu sabala vipacho pazelu ya mbuye watu Yesu Kristo. 9Nambo aliyese walibe vindu ivi wavio na vindu vapafupipe; iye ndisapenya. Waiwala kuelesendwe ndimachimo yake yakale.10Pa icho , abale wanga, chitani chili mbikilo ili kujilimbicha kusangindwa ndi kuitandindwa panjila yatu. Ngati simuchinte ngati simuchite yaya, simuji kuwala. 11Chocho simujipezele unyinji wa makamo yalowela ufumu wa muyaya pa mbuye watu ndi chiombolelo chatu Yesu Kristo.12Paicho ine sindikale okonjeka kukumbucha vindi ivi kila ndawi ata ngati muyajiwa , ndi sopano muli olombikila pa uzene. 13Ndikyaniza kuti ndili okonjeka bwino kwaucha ndikwa kumbuka kupitila vindu ivi, mikali nili mnyumba ino. 14Ndiposo ndijiwa kuti sindawi yaitali sinichoke nyumba yanga ngati ambuye Yesu Kristo umo adanilangizila. 15Sindijitaidi kojituma pandande yanu kuti mukumbukile vindu ivi pambuyo paine ndikuchoka.16Pakuti ife sitidachoche ndambo izo zidalovyedwa ndi ubwino paja tidali kufutokozela pamwamba pambavu ndi kujikulupililicha pambuye watu Yesu Kristo kuti ife tidaliu maumboni pachilungamo wake. 17"Iye wadalandila chilungamo ndi ulemu kuchoka pa Mulungu ambuye paja kuitanidwa kudaveka kuchoka pakati pachilungamo chachikulu kamba" uyu nde mwana wanga okodwa wanga yomwe nakondedwela naye. 18Tidavela mau yaya yachoka kumwamba paja tidali naye pafapapili poyela.19Titinalo ili mau la ulosi lidakululu pilika, pakuti mwachita bwino kuliko ja ndi ngati nyali iwalayo padima mbakana umawa nndi ndondwa zammalenga kucha zionekelazo pa mitima yanu. 20Mukumbukile yaya yakuti palibe ulosi uwo ulembedwa pa ndande ya kujiganizila pa mlosi mwene. 21Pakuti palibe mlosi udabwela pa chikondi chaife wandu, osakale wa ndufe tidakonjedwa ndi Mzimu Woyela adakamba kuchoka pa Mulungu.

Chapter 2

1Olosa aunami adatulukila kwa Aisraeli ndi apuzisi aunami nao sabwele kwanu. Kwa chisisi ndi kubwelesa mayaluzo ya unami, ndipo samkane ambuye adawa gula ajiwanangila achinawene mwa msanga. 2Ambili saachate njila zao za nchoni ndi kuitukwana njila ya zene. 3Kwa chipili saayamwe wanthu kwa mau ya unami, chilango chao sichichedwa kuwanangidwa kuchatika.4Kwa icho Mulungu siwadayembekeze angelo yao adang'anamuka wadaataya kwa wanthu akufa kuti amangidwe vingwe mbaka yapo chilango chao sichiabwelele. 5Ingakale Mulungu siwada yembekeze jiko la kale, adamsunga Nuhu pamoji ndi wina saba yapo wadasiilila maji yofulikila. 6Mulungu analapicha miji ya Sodoma na Gomora adaiwananga ndi kukala choso, kuti ikala ofyelo la ochimwa pa siku za mchogolo.7Pochita limenelo adampulumucha Lutu iye wamadandaulila wanthu amene saa matamande Mulungu. 8Ndande iye wamakala nao siku ndi siku wamapweteka mtima chifuko cha yaya wamagavela ndi kuyaona. 9Kwa icho ambuye ajiwa kupulumucha wanthu wake nthawi ya mavuto ndi kuyembekeza pa chilango cha ochimwa sikulotela.10Ichi ndi chilungamo kwa yao aendekela kukala ndi kumbilo la tupi ndi kupepula malamulo, wanthu amtundu uu ali ndi machili mmachimo yao, saopa kuatukwana oyela. 11Ingakale angelo ali mphavu kuposa wanthu saakoza kupeleka chilango cha o chimwawa kwa ambuye.12Nampho zinyamazi zopande njelu zako njedwa ndande yogwilidwa ndi kupedwa. 13Apwetekedwa mwa mphoto ya machimo yao usana wa mphuphu alongezeka ukadili ndi kukondelela chimyengo ndi iwe. 14Maso yao yavinikilidwa ndi chiwelewele saakwalanika kuchita machimo, anyenga ndi kuagwecha ochatila ateta, mmachimo alindi mitima yojala kumbilo ndi wana olesedwa.15Aleka njila ya zene achata njila ya Balaam mwana wa Beori, uyo wamakonda malipilo yo dwelela wanthu. 16Nampho wadamnyindila chifuko cha kula kwa kwake bulu iyo siimakambe idakamba ngati munthu, idachekeleza msala wa olosa.17Wanthu yawa ngati maji yofulikila popanda maji, ngati mitambo yachochedwa ndi mphepo, mtambo olemela wasungidwa ndande yao. 18Akamba kwa madama nditu, agwecha wanthu kwa kumbilo la tupi, omanyenga wanthu omena ayesa kutakwa wanthu ochimwa. 19Akuhepilicha wanthu mtendele nyengo achina wene akapolo amachimo.20Iye wajiika kutali ndi ukadili wa jiko kwa malango ya ambuye ndi mpulumusi Yesu Kristo ndi kubwelelacho ukadili sogolo lake likala loipa kuposa mmayambo. 21Mbasa wanthuo sadakajiwa ya uzene kulekana ndi kuijiwa ndi kuyasiancho matau ko adapachidwa. 22Mkambo wakalawa uzene kwao. "ndi nkhumba yochukidwa yabwelela kuwalauka mmatokope".

Chapter 3

1Chipano nikulembela, iwe, okondedwa iyi kalata ya kawili kuti kukuucha mnjelu, 2kuti mkose kukumbukila mau yadanenedwa mbuyo ndi olosa oyela ndi kukuza malamlo ya ambuye watu ndi mpulumuchi kwa kwatumila otumidwa.3Ujiwe kuti poyamba kuti oyipa siaje pakati pa siku zotela kukuchifilani voipa anyiimwe, niapita ngati kufuna kwao. 4Ndi akakamba chilikuti chikulupi cha kubwela? Achatale watu adafa nampho vintu voche vidali chimwecho chiyembile mmayambo mopanga.5Adajichita kuiwalila kuti jiko ndi kumwamba zidayamba kuchokelana ndi maji ndi kupitila maji kale la kale, mau la Mulungu. 6Ndi kuti kupitila mau lake ndi maji yadakala jiko kwa ntawi imeneyo ikakala yajhala maji, idawanangidwa. 7Nampho chipano kumwamba ndi jhiko zakuzikidwa ndi mau limwelo limwelo kwa chifuko cha moto. Vaikidwa chifuko cha siku ya malamulo ndi kuwanangidwa kwa wanthu osati wa Mulungu.8Iyi sikozekana kutawa utenga wanu, okondedwa kuti siku limoji kwa ambuye ndi ngati vyeka elfu imoji. Ndi vyaka Elfu Imoji ndi ngati siku limoji. 9Osati kuti ambuye achita pang'ono pang'ono kumalizila ngati imo iganizilidwa kuti nampho iye ndi oyembekeza ndi fuko chanu, iye siwakumbila ata mmoji wawanangidwe, Nampho kukumbila kuchocha ntawi kuti wonche apeze kulungama.10Ingakale siku ya ambuye siije ngati mghungu, Kumwamba sikupite ndi kuchita mapokoso. Vintu sivipwelele ndi moto. Jhiko ndi vintu vonche vilimo vivunukullidwe padanga.11Pakuti vintu vonche vipyelezedwe pa njila iyi, bwanji? Siukale muntu wa mtundu wanji? Ukale oyela ndi ukalo wa Chimlungu. 12Ifunika kujiwa ndi kukoza msanga kujha kwa siku ya Mulungu. Siku limenelo kumwamba sikupelezedwe ndi moto. Ndi vintu sivisungunichidwe ndi kufunda kokalipa. 13Nampho kuchokana ndi chikulupi chake, tilindilila kumwamba kwa chipano ndi jiko la chipano, ndipo yapo ovemelezekasiakale.14Kwa icho okondedwa pakuti tikulupalila vintu ivi limbikila kukala oganize ndi osada ndaulidwe ndi kukala ndi ntendele pamoji ndi iye. 15Ndi panyelela chiyembekezo cha ambuyatu pachimulumuchi, ngati okondedwa ochimwene watu Paulo, umo adekulembelani anyiimwe kuchokana ndi ulemu uwo adapachidwa. 16Paulo wakambilila yameneyo yonche pa kalata zake, kuli vintu volimba kuvizindikila. Wantu osakala ndi ulemu ndi chichimichimi awananga vintu vimenevo. Ndi ngati umo achitila mmalembo. Kupitila mawanangidwe yao.17Mmwemo okondedwa pakuti muyajiwa yameneyo, jisungeni mwachinawene kuti masalakwichidwa ndi kunyengedwa kwa onyenga ndi kutaya chikulupi. 18Nampho kutani ndi neema ndi kujiwa kwa ambuyatu ndi mpulumuchi Yesu Kristo. Ndi chipano ubwino uli ndiine chipano ndi kuendekela. Amina.

1 John

Chapter 1

1Chijha chidalipo kuyambila mmayambo chijha tidachivela chijha tidachiwona kwa maso yatu, chijha tidachipenya , ndi manja yatu yachigwila - Kukuza mau la umoyo. 2Ndi ujha umoyo udachitidwa kujhinoikana pa danga, ndi tauwona ndi kuwandikila, ndi kuwalandikila umoyo opitilila uwo udali kwa atate di udachitidwa kuhulikana kwa ife.3Chijha tidachiona ndi kuchivela tichilalikila kwa anyiimwe namwe kuti mkoze kusoganika pamojhi ndiife ndi ugwilizano watu pamojhi ndi atate ndi Mwana wake Yeu Kristo. 4Ndi tikulembelana vochitike ivi kuti anyiimwe chiwemwe chatu chivale chokwanilicha.5Uwu ndiwo utenga tidauvela kuchokela kwa iye ndi kuwalalikila; Mulungu ndi dangatila ndi mkati mwake mlibe ndima ata pang'ono. 6Ngati tikanena kuti titinichigwilizano ndiiye ndi tiyenda mdima tinyenga ndi sitichita vazene. 7Nampho tikayenda pa dangalila tigwilizana ife kwa ife, ndi mwaziwa Yesu Kristo mwana wake. Itichuka kuchokela kumachimo yonche.8Ngati tikanena tilipe machimo tijinyenga tachinawefe, ndi zene silinao mkati mwatu. 9Nampho tikayilapa machimo yatu, iye ndi okulupalika ndi malinga kutilekelela machimo yatu ndi kutichuka ndi yoyipa yonche. 10Tikanena kuti sitidachite machio timchita iye kuti waunami ndi mau lake sili mkati mwatu.

Chapter 2

1Wanawanga okondedwa nikulembelani nkani izi kwanu dala msadachita machimo nampo ngati mmoji wanu wakachita machimo tilinaye mtetezi walipamoji ndi atate Yesu Kristo mwe wali ndi vichito vabwino. 2Iye ndi woilanicha machimo yatu ndi osati kwa machimo yatu yoka nampo kwa jiko lampumpu. 3Kwa ichi tijiwa kuti timjiwa iye, ngati tikayosunga malamulo yake.4Iye wakamba, "ndimujiwa Mulungu" nambo wawayagwira malamulo yake wantila ndi uzene pavijemo mkati mwake. 5Nampo waliyenche waligwira mau lake zene pakati pamuntu mmeneyo chikndi cha Mulungu chili bwino, pakati palimeneli tijiwa kutili mkati mwake. 6Iye wakamba wa lama mkati mwa Mulunguifunika mwene wake wake wajiyendo ngati umo wayendela Yesu Kristo.7Okondedwa sindikulembelani anyiimwe lemulo lachapano ikapanda lamulo lakale limenelo mdelinalo chiyambilepo lamulo lakale nde mau limenelo mdalivela. 8Mmwemo ndikulembelani anyiimwe lemolo la chapano limenelo lazene pakati pa Kristo ndi anyiimwe chifuko mdima upita ndi kwa zene kuli tayari kuwala dangalile.9Mwene wakamba kutiwali dangalila nampo wamuipilambale wake wali pandima mpaka chapano. Mweve wamkonde mbale wake wali pandima mpaka chapano. 10Mweve wamkonda mbale wake walame padangalila ndipalibe nkani iliyonche ikoza kuwechanche. 11Nampo mmene wamwipila mbale ake wali pandima ndi waende kumdime, iye siwajiwa kuti wapita chifuko mdime watimicha maso yake.12Ndikulembelani anyiawe akondedwa chifuko wapurumichidwa machimo yanu chifuko cha jina lake. 13Ndikulembelani anya atate chifuk mumjiwa iye wadalipo chiyambilepo ndikulembelani anyamata chifuko mwanu wina oipa nakulembelani anyaimwe wana chifuko mumjiwa. 14Nakulembelani anyiimwe anya atate chifuko mumji wa iye wadalipo chiyambilepo nakulembelani anyaimwe anyamata chifuko mwaime ndi mau la Mulungu ndimane la Mulungu likale mkati mwanu ndi mu wina yuja oipa.15Msadali konde jiko ingakale ya mene yali mjiko ngati siwakalepo wali kondajiko, chikondi chakumkonde tate sichikalapo mkati mwake. 16Chifuko chilichonche chili mkati mwajiko vo funa vatupi vo funa vamaso ndi mwinya ya malamidwe sirichokela ndi atate nambo vichokele ndijiko. 17Jiko ndi vofuna vke vipita ikapande mmene wa chita vofuna Mulungu imeneyo sikale vyake vonche.18Wana waang'ono ndi ndi ntawi yotela ngati mmene mdevela kuti wochucha Kristo walimkuja mpakana chapano chucha Kristo afika kwa mtundu uu tijiwa kuti ntawi yotela. 19Adapita kuchoela kwato chifuko siadali wakwatu ngati akadekale akwatu akada endekale kuala pamoji nafe, nampo yapo adepita chimene chidejilangiza siadali akwatu.20Nampo mwapulupusidwa mauta ndi yuja walije machimo ndi mwawonche muujiwa uzene. 21Sindide kulembeleni anyiimwe chifuko simjiwa uzene ikapanda chifuka mumjiwa ndi chifuko palibe unami wauja uzene.22Yani waliwaunami ikapande mmeneyo wakanila kuti Yesu ni Kristo? 23Palibe wamchuche mwane wakale nditate ndi waliyenche wamvemelo mwana wali ndi atate.24Ngati kwa jifuko chanu mdachivela kuyambila mmayambo chisiyemu chiendekele kukale mkati mwanu ngati chija chivekela kuyambila mmayambo sichikale mkati mwanu so nincho simkale mkati mwa mwna wa atate. 25Mdali ndi pangano limene wadali pacha ife ufuru wa sata. 26Nakulembelani yaya anyaimwe kupitila anyiwaja mwa achogolelo anyaimwe pakati pa kutaika.27Ndichifuko chanu yaja mafuta mdalandila kuchokela kwaiye yakala mkati mwanu ndi simuyafuna. Muntu waliyonche kkuyaluzani ikapande ngati mafuta yakuyamzani kupitila nkati zonche ndi yauzene ndi osati unami ndi atangati mwato yalozidwa mkale mkati mwake. 28Ndichapano wana okondedwa mkale mkati mwake dala kuti yapo siwachokele tikoze kukale ndi olimba isatincho kujuue cha manyazi pachogolo pake pakati pakubwela kwake. 29Ngati mujiwa kuti iye ndiwazene mujiwa kuti waliyenchewachita uzene wali ndiiye.

Chapter 3

1Onani ndi chikondi cha mtundu wanji ambuye atininkha, kutititanidwa wana Amlungu ndi chimwechi ndimotili pa nande iyi jhiko silitijhiwa ife pakuti siudamjiwe iye. 2Okondedwa ife chipano ndi wana Amlungu ndi sidajiwike ikali umosikhali, tijhiwa kuti Kristu yapo siwaone, sitilingane ndi iye, pakuti sitimuone ngti umo wali. 3Ndi waliyonche uyo wali ndi chiyembekezo iche pakati pa nyengo ikuja yovemelezeka kwa iye wamang'anamuka kukhala oyera ngati iye umo wali oyera.4Wayonche uyo waendekela kuchita machimo watyola lamulo, ndande machimo ndi kutyola lamulo. 5Mjiwiwa kuti Kristo wadaoneka kuja kuchocha machimo ndi mkati mwake mulije machimo. Palije waliyonche wakala mkati mwake ndi kuyendekela kuchita machimo. 6Palije waliyonche wakala mati mwa machimo ikakala wamuona kapena kumjhiwa iye.7Wana okondedwa, msavomela kunyengedwa ndi munthu waliyonche, wachita chilungamo ndi wachilungamo, ngati Kristo naye umo wali wa chilungamo. 8Wachita machimo ndi wasatana ndande satana ndiwochita machimo chiyambilipo ndande iyi mwana wa Mlungu wadaoneka kuti wakhoze kwaiwananga nchito za satana.9Uyo wabadwa ndi Mlungu siwachita machimo ndande mbeu ya Mlungu ikala mkati mwake. Siwakoza kuendekela kuchita machimo ndande wabadwa ndi Mlungu. 10Pa ili wana Amlungu ndi wana asatana ajiwikana waliyonche wachita chosati chachilungamo, osati wa Mlungu, ndi uyo siwamkonda mbale wake.11Pakuti uwande utenga uko mudawela chiyambilepo, kuti ifunika tijikondana ife kwa ife. 12Osati ngati Kini wadali wa satana ndi wadampha mbale wake, ndi ndande chiyani wadampha? Ndanda vichito vake vidali voipa, ndi yija mbale wake wadali wa chilungamo.13Achabale wanga msazizwa, ngati jhiko likakuiphilani. 14Tijiwa kutidatotulukame mnyefa kulowa mu umoyo wa muyaya, ndande takonda mabale, waliyonche walije chikondi wakala mkati mwa nyifa. 15Munthu waliyonche kamuiphila mbale wake ndi wakupha, ndi wakupha umoyo wa muyaya siukhala mkati mwake.16Mkati mwailitijiwa chikondi ndande Kristu wadachocha umoyo wake ndande ya ife, ndi ife ifunika kujichocha ndande ya mabale. 17Nampho waliyonche wali ndi vinthu, ndi mbale wake wamuona osanka, nampho wauchekeleza mtima wake wa lisungu ndande yako, bwanji chikondi cha Mlungu chikala bwanji mkati mwake? 18Wana wanga okondedwa, tisaonda pa milomondi mau ya chabe ikapanda pa vichito ndi uzene.19Pa ile tijiwa kuti ifetili ndi uzene, ndi mitima yathu ioneka mkati mwaiye. 20Ngati mitima yathu ilamula, Mlungu ndi wa mkulu kuposa mitima yathu nde iye wajhiwa zonche. 21Okondedwa, gati mitima yathu siilamula tili opande mantha kwa Mlungu. 22Chalichonche sitiphomphe sitilandile kuchokela kwa iye, ndande tigwila malamulo yake ndikuchika zo mkwendwecha pamaso pake.23Ndi ili nde lamulo lake kuti tifunika kukulupalila pa jhina la Mwana wake Yesu Kristo ndi kukondana ife kwa ife ngati umo wadatilamulila. 24Uyo watemekeza malamulo yake wakala mkati mwaiye, ndi Mlungu wakhala mkati maiye. Ndipa ndande iyitijika kutiwa khala mkati mwathu, pa uja mzimu wadathininkha.

Chapter 4

1Okondedwa msidakulpalila kila mziu, nampho esani mzimu muone ngati zichokana ndi Mulungu, kwachifuko olosa ambili amtila achokela kujhiko. 2Kwa ili mjiwa mzimu wa Mulungu, kila mzim uo siuvomele kuti Yesu Kristo waja kupitila tupi ni ya Mulungu. 3Ndikila mzimu wasiuvomela Yesu osati ya Mulungu uu ni mzimu wakuchekeleza ambayo iyomdaivela kuti ikuja ndi chipano tayali ili kujikho.4Anyaimwwe ni Wamulungu, wana okondedwa, ndi mwatokwashinda kwa chifuko iye wali mkati mwanu ni wamkulu kuliko iye wali pajhiko. 5Anyiio ni apajhiko, kwachimwechoichoachikamba ni chapajhiko, ndi apajhiko avechela. 6Ife ni Amulungu iye wamjiwa Mulungu wativechela ife, iye osati wa Mulungu siwakoza kutivechela kupitila ili tijiwa mzimu wachilungamo ndi mzimu wa mtila.7Okondedwa, tikondane ife kwa ife pakuti chikondi ni cha Mulungu, ndi kila mmoji wakonda wabadwa ndi Mulungu ndi kumjiwa Mulungu. 8Iye siwakonda siwamjiwa Mulungu kwa chifuko Mulungu ni chikondi.9Kupitila ili chikondi cha Mulungu lidavunukulidwa mmitima mwathu, kuti Mulungu wadamtuma mwana wake wa yokha kujikho ili tilame, kupitila iye. 10Kupitila ichi chikondi, osati kuti tidamkonda Mulungu nampho iye wadatikonda, ndi wadamtuma mwana wake wakate faida kwa machimo yathu.11Okondedwa, kakala Mulungu wadatikonda ife, atachimwecho ifunika tikondane ife kwa ife. 12Palibe hata mmoji uyowadamuona Mulungungatitikakandana ife kwa ife. Mulunguwakala mkati mwathu ndi chikondi chake chakwanila mkati mwathu. 13Kupitila ili tijiwa kuti tikala mkati mwake ndi iye mkati mwathu, kwachifuko watipacha mzimu wake. 14Ndi tapenya ndi kushudia kuti Ambuye amtuma mwana kukala mkombozi wa pajhiko.15Kila uyowalapa kuti Yesu ni Mwana wa Mulungu wakala mkati mwake ndi iye mkati mwa Mulungu. 16Ndi tijiwa ndi kuamini chikondi icho walinacho Mulungu mkati mwathu, Mulungu ni chikondi ndi yewakala mkati mwa chikondi wakala mkati mwa Mulungu, ndi Mulungu wakala mkati mwake.17Kupitila chikondi ichi latakukamilishidwa kati yatu ili tukale ndi kujiami sikula lamulo, kwa chifuko ngati iye umowal, ndi ife ndeumotili katika jhiko lino. 18Palibe mantha mkati mwa chikondi, nampho chikondi chamate kuyataya mantha kubwalo kwachifuko mantha yahusiana ndi lamulo. Nampho iye waapa siwadakamilishidwe kupitila chikondi.19Timkonda kwachifuko Mulungu wadatikonda uti. 20Ikakala mmoji siwakambe, "Nimkonda Mulungu" nampho wamuipila mbale wake, niwamtila. Kwa chifuko uyo siwamkonda mbale wake, uyowamuona siwakoza kumkonda Mulungu ambae siwadamuone. 21Ndi ii nde amri iyotilinayo kuchokela kwake walienche wamkonda Mulungu wafunika kumkonda mbale wakenayo.

Chapter 5

1Waliyonche uyo wakomela kuti Yesu ni Kristo wabadwa ndi Mulungu. Ndi waliyonche wamkonda iye wachoka kwa atate nae wakonda wana wake. 2Kwaili tijhiwa kuti takonda wana Amulungu yapotimkonda Mulungu ndi kuvomeleza malamulo yake. 3Umu ndeumo timkondela Mulungu kuti tiyagwila malamulo yake. Ndi malamulo yake yopepuka.4Pakuti kila uyowabadwa ndi Mulungu walishinda jhiko. Ndi uku nde kukhoza kwa kulikhoza jhiko, chikhulupi chathu. 5Ni yani wadalishinda jhiko? Ni yujha wavomela kuti Yesu ni Mwana wa Mulungu.6Uyu nde uyowadajha kwa mwazi ndi majhi Yesu Kristo. Siwadajhepe kwa majhi nampho kwa majhi adi mwazi. 7Pakuti kuli atatu ashuhuda; 8Mzimu, majhi ndi mwazi. Anyiyawa atatu avomelezana.(Penyelela: mau yaya, "Atate, Mau ndi Mzimu Oyela" siyaonekana pakati pa nakala za bwino za kale).9Ngati tikulandila kuvomela kwa binadamu kuvomela kwa Mulungu ni wamkulu kupitilila. Pakutikuvomeleka kwa Mulungu ni uku - kuti walinako kuvomeleka kukhuzana ndi wana wake. 10Iye wamvomela Mwana wa Mulungu wali ndi umboni mkati mwake mwene. Ndi waliyonche uyosiwamkomela Mulungu wachita kuti wamtila, pakuti siwadauvomele umboni uo Mulungu waupeleka kukhuza mwana wake.11Ndi umboni nde ku - kuti Mulungu wadatipacha umoyo wa muyya, ndi umoyo uu uli mkati mwa Mwana wake. 12Uyo walinae mwana wali ndi umoyo. Uyo walibe mwana wa Mulungu walibe umoyo.13Nakulembelai yaya mukhoze kujhiwa kuti mulinao umoyo wa muyaya - anyaimwe muvomela pakati pa jhina la Mwana wa Mulungu. 14Ni uu nde uhasili uo tilinao pachogolo pake, kuti ngati tikapempha chinthu walichonche sawa sawa ndi chikondi chake wativechela. 15Ni ngati tijhiwa kuti wativela - walichonche tipempha tijhiwa kuti tilinacho icho tapempha.16Ngati munthu wamuona m'bale wake wachita machimo yayosiyapeleka nyifa, wafunika kupempha ndi Mulungu siwampache umoyo. Nikamba kwa anyiwajha machimo yao ni yajha siyapeleka nyifa - kuli machimo yampelekela nyifa - sinikamba kuti wafunika kupempha kwa chifuko cha chimo limenelo. 17Uasi onche ni machimo - nampho kuli chimo ilosilipeleka nyifa.18Tijhiwa ya kuti uyowabalidwa ndi Mulungu siwchita machimo. Nampho uyo wabalidwa ndi Mulungu wasungidwa nao mtendele, ndi yujha oipa siwakhoza kumpweteka. 19Tijhiwa kuti ife ni Amulungu ndi tijhiwa kuti jhiko lonche lilipanchi pa utawala wa yujha oipa.20Nampho tijhiwa kuti mwana wa Mulungu wajha ndi watininkha kujhiwa, kuti timjhiwa iye wali wa zene ndi kuti tili mkati mwake iye wali wzene, ata pakati pa mwanawake Yesu Kristo. Ndi Mulungu wa zene wa muyaya. 21Wana okondedwa, jhipembenuzeni ndi chifanifani.

2 John

Chapter 1

1Kuchoka kwa mdala kupita kwa wamkazi ochagulidwa ndi wana wake, anyiawo ni wakanda kwa uzene wala siyo inepee, nambha kwa anyiwaja ajiwa uzene, 2Ndande ya uzene uwo ulipo mkati Mwanthu iyosiikhale ya lama pamaji ndiii chiyambile kale. 3Neema kulekelela, mtindele sizikhale nae kuchaka kwa Mulungu tate ndi kuchoka kwa Yesu Kristo, Mwana wa atate kupitila Ulene ndi Chikondi.4Ndili ndi Chisanga lalo cha chikulu kuona kuti kuli wana aenda njila ya Uzene , ngati chichija tidalandila lamula kuchoka kwa utate. 5Chipano ndi kukambilaiwe, wamkazi osati kuti ndi kulembela lamula la chipana, nambha yaja tidali nayo kuchakila mmayamba kuti ifunikana tiji kondana ife kwa ife ndi ichi ndi chikondi tufunika kupita, kuchakanandi lamula lake. 6Ili nda lijalamula, ngati umo mdali velelakuchokale Mmayambha, kuti ifunikana kupita ndi ya manoyo.7Pakuti anyonga ambili ajala mjikho, ni savomela kuti Yesu Kristo wadaja kupila mtupi; uyunde wanyenga ndi siwavamdalana ndi Kristo. 8Mjipenye Mwachinawene kuti simtaiza vichita vija tidantho vichitila nchito, chipana ili kuti Mkhoze kuilandila mbhaso ya kwanila.9Waliyonjha uyowaendelea Mchagoro ndi si walimba kupitila ya luzo la Kristo, walibe Mulungu. Uyo walimba kupitila Mayaluzo wali ni atate ndi Mwana. 10Ngati Munthu wakuja kwanu ni siwapeleka yaluzo ili, simda mlandila mmakama Mwanu ni Simda mlanjela. 11Pakuti uyo wamlonjela waguilizana ni vichita vake vachimo.1213Nili ni vindhu vya mbili vya kukulembela, Ndi Sinidafune kukulembela kwa karatasi ndi wina ila ni khulupalila kuja kwanu ndi kukamba Masa kwa masa, kuti Chisenga la lo chatu chipate kuchitindwa ko kwanila. Wana wa dada wanu achagulidwa akulonjelani.

3 John

Chapter 1

1Amdala kwaagayo okondwendwa pauzene. 2Okondendwa ndikupempala kutimpeze ueneleliwampavu zabwino ngatimtima wanu umene upezela 3chifukwa ndida Kondwela kupunde ntawi ndeida ka mbidwila ndiabale wanga adabwele ndikuchoche yade chitika pamwamba pauzene wako ngati mmene muyendela pauzene. 4Ndilije chikondwe lelo chambili kupunda ichi kuvecha kutiwana wange aende pauzene.5Okondwendwa uendekele kwa chikulupi pamene mwa atandize abale ndi a lendo. 6Acheameneo achocho yo chitika pameso ya nyumba ya Mulungu uchitandabwino kwaachongoza kwanjila imeneyo imkondela Mulungu 7chifukwa cha Mulungu adepita posa tenga chilichonche kuchokela kwa wantu ameneo siamjiwa Mulungu. 8Kwaicho tifunike kuwa lalika wantu ngati ameneo dala kuti tikale ndiotandi zanao nchito cfhiukwa chauzene9Ndinde lilembela jiko wantfu adelipo mau la kutfi nammpo Diotrofe wako ndo kukole Muntu Oyamba mmoja muwa wantu adelipo si wa movanenao. 10Kwaicho nikabwela sindi ya kumbu kile yo chita yake waja chita ni mmene waja nenela mau yoipa kumbuyo nope siwa da kubwele ndivo chita ivi iye mwene wake siwa wa lendila alendo mmwemo wa kanize weno ameneama kumbila kuwalandile olendo acho abale ndi kwa ato pole achoke mketi mwau11Okondweda usade ya chata yaliyoipa uya chate yali ya bwino mmene wa chita yabwino ndi wa Mulungu wa chita yoipa siwande mwone Mulungu. 12Demetrio wadekeibwila ndioche ndile zene wake ie nefechu ndimboni ndi ujiwa kuti udato kamb idwila uzene watu wa uzene.13Ndili ndi zochita za mbili kukulembela kwa malembo ya chole mbela. 14Ikapanda ndikulupalila kupezena na we posh chedwapa ndisiti kambi lare moso kwamoso. 15Mtendele ukale nawe mabwenji akulonjela kwa maineyao

Jude

Chapter 1

1Yuda Kapolo wa YesuKristo, ndi m'bale wake Yakobo kwa anyiyao atanitwa okondendwa ndi ambuye mulungu atate yao asungidwa kwa ndande ya Yesu Kristo. 2Lisungu ndi mndele ndi chikondi vikuchogoleleni kwanu.3Okondendwa, nyengo iyo nimachita chokozeka kulembelani anyaimwe kukhuza chipulumusi chatu taonche, nidafunika kulembelani kwa chifuko cha kukushaulini muyambanile pa ntendele iyo idaninkidwa mala kamoji pendi yao aamini. 4Kwa chifuko wanthu wakuti ajilovya kwa chisisipakati panu - wantu anyiyao adaikidwa chidindo cha chilango - wanthu anyiyao sadaele anyiyao ang'anamula neema ya Mulungu watu kukala unkungu, kwa kumkana Mulungu watu ndi Yesu Kristo.5Chipano nikonda kujimichani anyaimwe ingakale kuti kuli nyengo mmajiwa bwino kuti Ambuye adawalamicha wanthu kuchokela mjikola Misri, nampo pambuyo pake wadawamanga anyiwaja osakulupalila. 6Ndi angelo anyiyao sadapenyelele nyengo yao achinawene nampo adasiya maloyao yokala Mulungu adawaika mvingwe va muyaya, mkati mwa mdima, kwa chilango cha siku ya ikulu.7Ngati muja Sodoma ndi Gomola ndi miji idazungulila, ndi idajilovyamo ene mkati mwa chiwelewele ndi adachata kumbilo lopande chiyambo adalangizidwa ngati mano ya anyiwaja ovutika mkati mwa chilango cha moto osata. 8Ingakale kwa njila imweija olosa adachecha matupi yao, ndi adaka malamulo, ndi kunena unami pakati pa oela.9Nampho ata Mikaeli angelo wa mkulu nyengo iyo wamanyambana ndi satana ndi kufunchana kwa chifuko cha tupi la Musa. Siwadaese kupeleka chilango cha unami pakati pake, nampho pambuyo pake, wadakamba ambuye akupalipile. 10Nampho wanthu anyiyawa apeleka unami pakati pa chinthu icho sachinjiwa. Ndi chija sachinjiwa - ndi chija ambacho zinyama zopande njelu ajiwikana kwa vichito ndi ya meneyo nde ya yo yawananga. 11Ole wao! Kwa chiuko aenda mnjila ya Kaini ndi kuchata kulakwa kwa Balaamu, adapwetekedwa mkati mwa kulakwa kwa Kora.12Anyiyawa ni myala pa chisangalalo chanu cha chikondi, asangalala popande nchoni, ndi kuja achinawepe. Ndi mitambo yopandemaji, yatengedwa ndi mphepo, ndi mitengo yopande machamba ndi vipacho iyoyamwalila kawili, iyo yazulidwa mizo. 13Ndi maunde ya nyanja yayoyapeleka mapokoso ya manyazi ya achinawene, ndi nthondwa izozizungulila zungulila zilindi mdima wakuda wasungidwa kwa chiuko chao muyaya.14Enoki wa saba wadalosa pakati pao anyaio, wadakamba, penya! Ambuye akuja ndi maelu ndi maelu ya wanthu wake oela, 15ili wachite chilango pakati pa kila munthu, nikutilani mmanja mwaonche osamkulupilila Mulungu pakati pa njila zosati zoela, ndi kwa mau yao yonche yokalipa osati oela wayakamba paka pake. 16Anyiyawa nde anyiwaja odadaulao, achata kumbilo la kulakwa kwao kwa volakwa kwa madama kupunda, anyiyao kwa mphoto zao wanamiza wina.17Lakini anaimwe, okondendwa kumbuki lani mau yayoyadakambidwa kale ndi atumiki wa ambuye Yesu Kristo. 18Adakamba kwa anyaimwe, "kupitila nyengo yo tela sikukale wanthu anyiyao amuesela anyiao alichata kumbilo lao lopande loela". 19Wanthu anyiyawa ndi opatulichana, atawalidwa ndi kumbilo la chiyambo.20Lakini anyaimwe, okondendwa, mjimange mkati mwa chikulupi chanu choela kupunda, ndi umo mpemphela Mzimu Oela. 21Jisungeni pakati pa chikondi cha ambuye, ndimulindilile ulemelelo wa ambuye watu Yesu Kristo uyo wa apacha umoyo wa muyaya.22Langizani mtendele kwa anyiwa ali ndi mantha. 23Alamicheni wina kwa kuwanyamula kuchoka pakati pa moto. Kwa wina langizani lisungu ndi kuopa, mkatengelelana ndi chovala ichochatilidwa chidindo ndi tupi.24Chipano uyawakuza kukupenyelelani msajikuwala, nikuchitani muime pachogole pa mtendele wake, papanda chidindo ndi kukala ndi chisangalalo, 25kwa Mulungu yoka mpulumusi kupitila kwa Yesu Kristo atate watu, ulemelelo ukale ndi iye, ukulu ndi mphavu nyengo zonche, ndi chipano mbakana muyaya. Amina.

Revelation

Chapter 1

1uu ndi mmasura wa Yesu Kristo amboo Mulungu wadamninkha ili kwaalangisa atumiki wake richito ambavo lazima vichokele kalibuni. Wadayachita ili uajuike kwa kumtuma angelo wake kwa mtumiki wake Yohana. 2Yohana wadachacha ushuhuda wa kila chinthu icho wadachina chihusu maula Mulungu ndi ushuhuda wo unda chochodwa kuhusu Yesu Kristo. 3Ulabaliki dwa ize wasoma kwa sauti ndi anyi wapa onche anyiyawo avela mau ya orasa uu nde kuvamela icha chalembedwa mmenema, kwa chifu kwa nyengo yakalibia.4Yohana, kwa nyumba za mapemphola saba izazili ku Asia: mwauli ukhale kwanu ndi mtendele kuchoka kwake uyowalipo, uyondalipo, ndi uyasi waje, ndi kuchoka kwa mizimu saba alipa chogolo pampando wake wa enzi, 5ndi kuchoka kwa Yesu Kristo ambaye ndi shahidi okhulupalika, obadwa oyamba waakufa ndi alamula wa mfumu wa jika ili. Kwakua iye wafikanda ndi wafika huru kuchaka pakatipa vachima vathu kwa mwazi wako, 6watuchita kukala afumu, achembe a Mulungu ndi a tata wake - kwake kukala chitukuka ndi mphavu muyaya. Ameni.7Penya, watokuja ndi mitambo; kila disa silimuone, pamoji ndi onche adamlasa. Ndi kabila zacheza pajiko sizipomphele kwake etu, Ameni. 8''Ine ndi Alufa ndi Omega, ''Wakamba mbuye Mulungu, ''Iye walipa, ndi wadalipo, ndi uyo wakuja, mwene mphavu.''9Ine, Yohana - mbale wanu ndi mmoji uyo wagwiliza pamoji namwe pakati pa matiso ndi ufuma ndi kudikilila kwa uzene uwo ulikupitia Yesu; ni dalipahati pa chilumbo chitani dwa patimo kwa chifukwa ya mmau la Mulungu ndi ushuhuda kuhusu Yesu. 10Ndidali kupitila mzimu siku ya ambuye. Ndidavola kumbuya kwanga sauti ya pamwamba ngati ya tarumbeta, 11ndiikamba, ''Lemba kupitila chitabu yaya uyaana, ndi uyatwume kwa nyumba za mapomphelo saba, kupita ku Efeso, kupita ku Smirna, kupita Pergamo, kupita Thiatia, kupita Sardi, kupita Philadelphia, ndi kupita ku Laodikia.''12Nidang'a na mukakuona ndi sauti ya yani uya wamakamba nane, ndi yaponidang'a na miuka ni daona kinara cha dhahabu cha taa saba. 13Pakati pa kinara cha taa wadalimo mmoji ngati mwana wa Adamu, wavala kanzu yaitari iyofika panchi pa myenda yake, ndi lamba la dhahabu kuzungulila chidale chake.14Mutu wake ndi machichi yake vidali vaela ngati sufu zaela ngati theluji, ndi maso yake yadali ngati chikuni maata. 15Vikhati vake vidali ngati shaba iyoyasugu lidwa sana, ngati shaba ambayo yatho pitichidwa pakati pa mato, ndi sauti yake idari ngati sauti ya maji yambili yayoyachikirila ka mphavu. 16Wadagwililila ntha ndwa saba pakati pajanjalake la kwene, ndi kuchaka ku kamwa kwake kudali ndi chikwanje chakutwa chili ndi kutwa kwiili. Pamaso pake padangara ngati dangolila likali la jua.17Yaponidamwona, nidanga na mukapamyenda poke ngati muthu uyowafa.Wadaika janja lake wa kwene pamwamba panga ndi kukamba, ''Usidaopa! Ine 18ndi oyamba ndi othela, ndiuyo ndi ishi. Ndidafa, nampha penya, ndiishi wamuyaya! Ndi nilinaza fungua za kufa ni kuzimu.19Chipano, yalembe yayo wayaona, yayoyalipo saina, ndiyaja siyachakele baada ya yaya. 20Pakuti ichochajibisa kuhusu nthondwa saba izo waziona kupitila janjalanga la kuchimuno ndi chija kinara cha dhahabu cha taa saba: nthondwa saba ndi angelo wa yaja manyemba ya mapemphela saba, ndi kinara cha taa saba ndi yaja manyumba ya mapenphelo saba.''

Chapter 2

1''Kwa angelo anyumba ya Mulungu ya ku Efeso lemba: 'Yaya ndi mau ya yuja wagwililila nyenyezi zisano ndi ziwili pa jhanja lake la kwene. Uyo waenda pakati pa ndodo ndi nyali zisano ndi ziwili za golide wakamba chimwe, '' 2''Ndijiwa icho wachichita ndi kulimbicha kwako pa nchito ndi kupilila kwako kosatepatepa ndi kuti siukhoza kugwilizana nao ali ochimwa, ndi waesa onche ajitana atumiki ndi kutinoto ndiaonekha kuti aunami.3Ndijhiwa uliolindilila ndi kulimba mtima, ndi wapitila za mbili ndande ya juna langa, ndi ukhali osalema. 4Izi ndeizo ndili nazo pakati paiwe, nampho wasia chikondi chako chayamba. 5Kwaicho kumbukila yapo udagwa, ukaungame ndi kuchita vichito viyamba. Ngati si ungama sindije kwawe ndi kuchocha ndodo ya nyali yako kuchoka pamalo pake.6Nampho iwe ulindi izi, uipila vjha adachita anikolai, ivo ata ine sindivikonda. 7Ngati uli ndi khutu, vechela yajha mzimu wakambila mipingo, uyo siwapambane ndiza mphacha lamulo la kudya vipacho va mumtengo wa umoyo uwo uli kuparadiso kwa Mlungu.8Angelo anyumba ya Mulungu a Smirna lemba: 'Vaya ndi mauyayujha oyamba ndi Othela uyo wadamwalila ndi kukhala ncho moyo: 9'''Ndijhiwa mazungo yako ndi kusauka kwako (nampho we ndi olemela) ndi unami wanyiwaja ajitana ayahundi (Nampho osati anyaio ndi mpingo wa satana).10Osaopa mazunjo yayosi ya kupheze. Penya! Satana wafuna kuaponya mndunde akumoji wa anyaimwe kuti mkhoze kuyesedwa ndi simzunjidwe masiku khumi. Khalani okhulupalika mbakana kumwalila ndi sindikhuninkheni mphotho ya umoyo. 11Ngati uli ndi kuthu, vechela mzimu icho ikambila mipingo uyo siwapambane siwafa nyifa ya kwili.'12''Kwa angelo anyumba ya Mlungu ya ku Pargamo lemba: 'Izi ndi izo izo wakamba iye uyo wali ndi shikwanje chokalipa chotema konke konche. 13'''Ndipajiwa pamalo yapoukhala, pamalo yapo uli mpando wa chifumu wa sarana. Atachimwecho iwe waligwila kupunda jhina langa, ndi siudachikane chikulupi chako chili ndiine ingakha pa masiku yaja ya antipasi mboni wanga okulupalika wanga, wadapedwa mkati kati mwanu pamenepo nde yapo wakhala sarana.14Nampho ndili vinthu vochepha pakati panu: Kumene uli ndi wanthu yao agwila mayaluzo ya Balaamu, iye wadamuyaluza Balaki kuchekeleza wana aku Israeli, kuti ajidya vakudya ivo vachochedwa nchemu kwa milungu yoipa ndi kuchita chigaldo. 15Chimojimoji, ingakhale iwe uli ndi akumoji wao agwila mayaluzo ya Anikolai.16Chipano lapa! Ngati siuchita chimwecho, ndikuja msanga, ndi sindiyambane nawp ndi chikwanje chochokela mkamwa mwanga. 17Ngati uli ndi kuthu, vechela icho mzimu ukambila mipingo, uyo siwapambane sindimninkhe mana ya kumoji iyo yabisika, ndi sindimninkhencho mwala oyera lalembedwa jhina la chiphano pamwamba pa mwala jhina ilo palike uyo walijiwa ikapanda uyo siwalilandile.'18''Kwa angelo anyumba ya Mlungu ya Thiatira lemba: ''Yaya nde mau ya Mwana wa Mlungu, uyo wali ndi maso yake ngati moto ndi maphazi ngati chichulo chowala: 19'''Ndijiwa icho wachichita - chikondi chako ndi chikulupi kutumikila kwanu ndi kulimbikira kwanu, ndi kuti ucho wachita pafupi yapha ndi kuti chambana kuposa chija udachita mmanyambo.20Nampho ndili ndi izi pakati pa iwe: wamulekelela wamkazi Yezebeli wajituna mwene mneneri wa mkazi, pa muyaluzo yake, wanamiza anchito wanga kuchita chigoldo ndi kudya chakudya chachochedwa nchemba kwa chosepa. 21Ndidamphacha nyengo yolapa, nampho siwada lapile uomboli wake.22Ona! Sindimtaye mmatenda, ndi anyiwaja achita za dama naye mmazunjo yokalipa, mwena mwake alape paizo azichita. 23Ndimenye wana wake kuti afe ndi mipingo yonche sajiwe kuti ine ndiye ndizondelela maganizo ndi kumbilo, sindimphata waliyonche kanu kujela vichito vake.24Nampho akumoji wanu yawo wakalila ku Thiatira, kwa wonche yawo sadagwile yaluzo ilindiyao sinjiwa chija akumoji atana mayaluzo ya satana, ndikamba kwanu pamwamba panu sindika katundu waliyonche.' 25Pa nkhani yaliyonche, khalani nganganga mbakana yaposindije.26Waliyonche uyo swapambane ndi kuchita icho ndidachita mbakana potela, iwe sindi mphache lamulo pakati pa wanthu amitundu. 27''Wazalamulila ndi ndodo ya chichulo, ngati mbale ya mbiya, siwatiyoletyole.' 28Ngati umo ndidalandilila kuchokela kwa kwa atate wanga, sindimninge ndi nyenye ya umawa.' 29Ukakhala ndi kuthu, vechela chija mzimu uikambila mipingo.

Chapter 3

1Kwa angelo wakanisa la Sardi lembe: 'Mau yayujha wagwililila ija mizimu saba ya Mulungu ndi nthondwa saba.'' Nijiwa ambacho wachita. Ulini sifa yakukala wamoyo, nampho u - mfu. 2Uka ndi kuimarisha yayo yakalila, nampho yako pafupi kufa kwachifuko siudawaone vichito vao vakamiliko pamaso pa Mulungu.3Kwachimwecho, kumbukila, yaja udayalandila ndi kuyavela. Yaulemu ndi kutubu. Nampho ngati siuuka, sinije ngati huli, ndi siujiwe nawi yanji iyo sinije pa mwamba pako. 4Nampho kulimajina yochepa ya wanthu katika Sardi ambapo siadachafue nchalu zao siaende pamoji nane, avala nchalu zoela, kwa chifuko astahili.5Iye siwashinde siwavekedwe vivalo vaela, ndi kamwe sinilifuta jina lake kuchokela katika chitabu cha umoyo, ndi sinilitaje jina lake pachogolo pa ambaye wanga, ndi pachogolo pa angelo. 6Ukakala ndi masikio, vechela mzimu wayakambila makanisa.''8''Kwa maongelo wakanisa la Philadefia lembe: Mau ya uyowalioyela ndi uzene - wali ndi funguo za dauchi, kuchakula ndi palibe wacheka, kucheka ndi palibe wakoza ku chakula. 7Nijiwa ambacho wachita, penya, nakuikila pachogolo pako chicheko ichochakulidwa ambacho palibe wakoza kuchakula. Nijiwa ulinazo mphavu pangono, napho watii maulanga ndi siudalikane jina langa.9Penyani! Onche alimmasinagogi la lasatana, inyiwaja akambao anyaiwo wayahudi ndi kumbe osati, pambuyopake anyenga. Sinachiteaje kumgwandilo pachogolo pa myendo mwanu, ndi si ajiwe yakuti ndikukonda. 10Pakuti wausunga lamulo langa kwa uvumilivu wa uzene, ndi sinikupenyelele kupitila nthawi yako ya mayeso ambayo ikuja kupitila jikolonche kuwaesa anyiwaja onche anyao alama kupitila jhiko. Nikujha chisangu. 11Gwililila sana chijha ulinacho ili wasadakhalapho munthu wakuitenga taji yako.12Sinimchite iye wakhoza kukala nguzo kupitilahe kalula Mulungu wanga, ndi siwachoka kubwalo kamwe. Sinililembe kwake jina la Mulungu wanga, ndi jina langa la chiphano. 13Iye wali ndi sikio, ndi wavele ambacho wakamba kwa nyumba ya Mulungu.'14''Kwa maangero wa nyumba ya Mulungu la Laodikia lembe: 'Mau yake wali Amina, amkhulu phalila ndi wakumuimilila oaminika, watawala. 15Nijiwa chilipho wachichita, ndi kuti iwe osatiwa ozizila wala wamoto, ndikumbila kuti udakhakala wa ozizila au wamoto! 16Chimwecho, kwachifuko ni mkamwa osati moto wala ozizila, sinikusanche kuchoka kukosi kwanga.17Pakuti ukamba, ''Ine nifuri, nakala ni chuma cha mbili, ndi funa chalichoche.'' Nampho siujhiwa kuti iweni fukala sana odandaulicha, fukala, thinyike ndi maliseche. 18Vachela ushauli wanga, gula kwanga alumasi iyo ya chikidwa kwa moto ili upeze kukala fulu, ndi nchalu zoela zo naelemeta ili uvale umwene ndi sidalangiza nchani yalisechelako, ndi mafuta ya kuphaka katika maso yako upate kupenya.19Kila nimkonda, nimuelekeza ndi kumuyaluzanjila ifumika kulama, kwachimwecho uzene ndi kumgwadila. 20Penya niima katika chicheko ndi kutimba hodi. Waliyenche wavela sauti yanga ndi kuchakula chicheko, sanije ndi kulowa mnyumba yake, ndi kudya chakulya naye ndi yepamoji nane.21Iye wakoza, sinimpache haki yakukala panchipamoji nane pamwamba pa mphando wanga waenzi ngati mujha ine nidakhoza ndi kukala panchi pamoji ndi ambuye wanga pamwamba pa mpando wake wa enzi. 22Iye wali ndi sikio, ndi wavechele chilipho mzimu wayakhambila makanisa.''

Chapter 4

1Pamalo pa vinthu ivi nidapenya, nidaona kuti chicheko chidachakulidwa kumwamba. Ijha sauti yoyamba, niikambana nane ngati tarumbeta, niikamba, majha pano, nikulangize yayosiyachokela pambuyo pa vinthu ivi.'' 2Mara kamojhi idali pakati pa mzimu, nidaona kudali mpando wa enzi waikidwa kumwamba, ndi munthu waukhalila. 3Mmojhi uyowadaukhalila ngati mwala wa yospi ndi akiki. Kudali ndi mtawaleza wa vula wauzungulila ijha mpando wa enzi. Mtawaleza udaonekana ngati zamaridi.4Kuazungulila mpando wa enzi kudali ndi mipando ya enzi injake ishirini ndi inai, ndi yao adakhala mmipando ya eni adali okotha ishirini ndi anai, avekedwa vovala voela ndi kolona za zahabu mmitu mwao. 5Kuchokela pa mpando wa enzi kudachoka miale ya mphambe, mitungulu ya mphambe. Nyali saba zimakwelela pachogolo pa mpando wa enzi, nyali zimenezo ni mizimu ya Mulungu.6Tena pachagolo pa mpando wa enzi kudali ndi nyanja, iyo idali wazi ngati gilasi. Onche kuzungulila mpando wa enzi kudali ndi amoyo anai, yaodajhala masokuchogolo ndi kumbuyo.7Chokonjedwa choyamba chamoyo chidali ngati mkango, chokonjedwa chakawili chidali ngati mwana wa ng'ombe, chokonjedwa chakatatu chidali ndi nkhope ngati ya munthu ndi yujha wa moyo wakanai wadali ngati thai opululuka. 8Vokonjedwa va moyo vinai kila mmojhi wadali ndi mapapiko sita, ajhala maso mmwamba ndi panchi pake. Usiku ndi usana salapa kukamba, oyela, oyela, oyela, ni ambuye Mulungu, olamula pakati pa yonche, uyowadalipo, ndi uyowalipo ndi uyosiwajhe.''9Kila nyengo vokonjedwa vya moyo yapoadacho cha ufulu, ulemu, ndi kuyamika pamaso pa uyowadakhala pa mpando wa enzi, iye walama muyaya ndi daima, 10okotha ishirini ndi anai adamgwadila achinawene pamaso pake uyo wada khalila mpando wa enzi ni kukamba, 11''Uvomeleka iwe, ambuye wathu ndi Mulungu wathu, kulandila ufulu. Ndi ulemi ndi mphapovu. Pakuti udavikonja vithu vonche, ndi kwachikondi chako vidalipo ni vidakonjedwa.''

Chapter 5

1Pambuyo pake ndidaona mjanja la kwene yuja wadakhala pampando wa chifumu chikalakala chalembedwa kuchogolo ndi kumbuyo, ndi chidadindidwa vidindo visano ndi vuwili. 2Ndidamwana mngelo wa mphamvu wamalali kila mokweza mau, yani waenela kuvunukwala chikalakala ichi ndi kutyela vidindo vake iui?''3Palije munthu kumwamba kapena pa jhiko kapena panchi pa jhiko wadakoza kuchimaswa chikalakala kapena kuchirenga. 4Ndida lila mowawamtima pakuti siwadasume anike waliyonche wamaenela kuchimasula chikala kala ndi kuchiwelenga. 5Nampho mmoji wa midala wadani kambila, usalila. Ona! mkango wa fuko la Yuda, chijukulu cha Daudi, wapambana, ndiwakho kuchima sula chikalakala ndi vidindo vake visano ndi vuwili.''6Pakati pa mpando wa chifumu ndi amoyo anai ndi mkati kati mwa midala, ndidaona mwana wa mbelele waima, wamaoneka ngati wapendwa. Wadala ndi nchiwazisano ndi liwili ndi maso ya sano ndi ya wili iyi ndi mizimu isano ndi wili ya Mlungu zatumizidwa pa jhiko lonchoe. 7Wadapita kutenga chikalakala kuchokela pa janja la kwene la yuja wadakala pa mpando wa chifumu.8Wadatenga chikalakala, amoyo anai ndi midala makumi ya wili ndi anai andakwatama mbakana pa jhiko pachogolo pa mwana wa mbelele, waliyenche wadali ndi zeze ndi mbale ya golide yojala lubani yayo ndi phemphelo ya wanthu a Mulungu.9Ankaimbila nyimbo ya chipano, uenela kutenga chikalakala ndi kuvimasula vidindo vake. Pakuti udaphedwa, ndi magazi yako udamgulila Mlungu wanthu amitundu yonche, mkambo ndi jhiko. 10Udaachita ufuma ndi anchembe ndande ya kumtumikila Mlungu wathu, nawonche sala mulile jhiko.''11Ndipo ndidaona ndikwela mau ya angela ambili kuzungulila mpando wa chifumu adali akwana 200, 000, 000 amoyo ndi midala. 12Adakamba mokweza mau, waenela mwana wa mbelele uyo waphedwa kulandila mphamvu, chuma, njelu, mphamvu, ulemu, ulemelele ndi chiyamiko.''13Ndida vela chilichonche icho chidalengedwa chidali kumwamba ndi pa jhiko ndi panchi pa jhiko ndi pa mwamba pa nyanja, chilichonche mkati mwake chimakamba, kwaiye wakala pa mpando wa chifuma ndi kwa mwana wa mbelele, kukhale chiyamiko, ulemu, ulemelelo ndi mphamvu yolamulila muya ndi muya.'' 14Amoyo anai adakamba, ''Amina!'' Ndi midala idagwada ndi kulambila.

Chapter 6

1Nidamuona mwana wa nkhosandiwamasula chidindo chimoji mwa vija vidindo saba, nidavela mmoji wa anyiwaja ali ndi moyo anai ndi wakamba kwa mkambo oluluma maja, 2''Nidapenya padali ndi buru oyera ndi uyo wadakwela baruyo wadali ndi uta wadapachidwa chisoti cha ulemu, wadachoka wapambana kuli wapambana nendo.3Ndi yapo wadamasula chidindo cha kawili, nidamvela yuja wali yuja wali ndi moyo wakawili niwakamba maja!'' 4Nidaona wadachokela buru mwina ofwila ngati moto. Ndi uyo wadakwela buruyo wadapachidwa lamulo lochocha mtendele pa jiko la panchi, kuti wanthu apane ndi wadapachidwa chikwanje chachikulu.5Yapo wadamasula chidindo cha katatu nidamvela yuja wali ndi moyo wakatatu, ndi wakamba maja!'' Nidaona buru wakuda, uya wadakwela buruyo wadali ndi kapani mmanja mwaka. 6Nidavela mkambo pakati pa ali ndi moya anaio, ndi ikamba chibaba cha ngano kwa ndi vubaba vitatu va kwa imoji nampho usayawenga mafuta ya mvinyo.''7Ndiyapo adamasula chidindo cha kanai nidavela mkambo wa yuja wali ndi moyo wakanai ndi wakamba maja!'' 8Nidaona buru wachoso choso, ndi uyo wadakwela bwuyo jina lake nyifa wamachatana ndi kumanda ada ninkhidwa lamulo la kupa wanthu robo ya jiko la panchi, ape kwa chikwanje, ngala, ndi vinyama vajiko la pa nchi vongangara.9Yapo wadamasule chidindo cha kasano nidaona panchi pa madhabao mizimu yao adadulidwa mitundande ya mau la Mlungu ndi ulaliki adali nao. 10Adalila kwa mphavu, ndi kukamba, ambuye mhingu oyera ndi uzene, mbaka chakanji simchodwe kulanga ndi kuulipa mwazi watu kwa yao akala jiko la panchi. 11Kila mmoji wadapachidwa nchalu yailali yoyera adakambidwa, alindile ikali nthawi pangono, mbaku yapo sukwanile nthawi pamene atumiki anjao ndi abale wao yapo saapedwe ngati umo adapedwela amjiiwo.12Yapo wadamasula chidindo cha sita nidaona padali chimtingiza chachikulu, jua lidali lakuda ngati saka mwezi udali afwila ngati mwazi. 13Nthondwa zidagwa panchi ngati mtengo umo upulusulita vipacho vake ivo si vidawkime, nyengo yamphepo yamphavu. 14Kumwamba kudachochodwa ngati kuvinikila kwa chikalakala, ndimapili ndi chilumba chida chochodwa pamalo pake.15Mafumu amjiko ndi wakulu akulu ndi aimilila asikali ndi achuma ndi alindi mphavu ndi akapolo ndi wachilungamo oadajibisa kungolo ndi panchi pa myala ya ikulu ya mpili. 16Adayakambila mapili ndi myala yaikulu tigweleni mtibise, pamaso iye wakala pa mpando wa ulamu ndi mphwai za mwana wa nkhosa. 17Mateyake, siku yaikulu, yabmphwai yao, yafika, yani wakoza kuima chiimile?''

Chapter 7

1Baada ya faya midaona angelo anai ama kuvisongwa vinai va jiko, akinga mpharo zinai za jiko kwa nnhongono dala kuti pasakala ndi mphepo yo puliza katika jiko, pamwamba pa bahari au pamato pamtengo walionchhe. 2Ndidaona angelo mwina wakuja kuchoka kuwuka kuvuma, wadalindi chidindo cha Mlungu wali wa moyo wadalila kwa sauti ya chidandaula kwa angelo amai anyiyao adapachindwa lamulo la kuliwamanga jiko ndi bahari: 3''Msaliwamanga jiko, bahari, au mitengo mpaka ya popikale tatoika chidinato katika mphumi za mitu ya otumika a Mulungu watu.''4Nidavela idadi ya anyiwaja aikidwa chidindo: 144, 000, anyiyao aikidwa chidindo kuchoka kila yuko la wanthu a Israeli: 512, 000 kuchoka katika yuko la Yuda adaikidwa chidindo, 12, 000 kuchoka katika fuko la Reubeni, 12, 000 kuchoka katika yuko la Naftali, 12, 000 kuchoka katika yuko la Gadi. 612, 000 kuchoka katika yula la Asheri, 12, 000 kuchoka katika la Naftali, 12, 000 kuchoka katika yuko la Manase.712, 000 kuchoka yuko la Simioni, 12, 000 kuchoka yuko la Lawi, 12, 000 kuchoka yuko la Isakali, 812, 000 kuchoka yuko la Zebuloni, 12, 000 kuchoka yuko la Yusufu, ndi 12, 000 kuchoka fuko la Benyamini adatihadwe chidindo.9Baada ya nkhani izi ndidapenya ndi kudali gulula likulu ambalo palija munthu qanda kakoza kuwelenga, kuchoka kila kamu jiko, fukoafamphepete, ndi mnambo - aima pachogolo pa mpando na ufala ndi pachogolo pa mpulumusi. Adali avala adhalu yoela ndi ali ndi matawi ya mitende mmanja mwao, 10Ndi adali atoma kwa sauti ya pamwamba kuombolelwa ndi kwa Mlungu iye wakala katika mpando wa afulu ndi kwa mpulumusi!''11Angelo adhe adali aime kuzungulila mpando wa ufulu ndi kwazungulila anyiwaja azee pamoji ndi ali ndi umoyo amai, ada kwatamo panchi panthaka ndi adaika nkhope zao pamwamba pa nthaka pachogolo pa mpando wa ufulu ndi pampha Mlungu, 12ndiakamba, ''Zene! Kuelekela ndi ufubu, njelu, kuyamika, kukoza ndi nkhongono vikali kwa Mlungu watu muyaya ndi muyaya! Zene!''13Nampho mmoji wa amyiwaja midala wadanifu nchha, ''Anyiyawa ndi achiyami avala kanzu yoela ndi achoka kuti? 14Ndidamnambila, ''Munthu wammulu, ujiwa uwe, ''Ndi wadanikambila, ''Anyiyawa ndi anyiwaja achoka katika vutola likulu Azichapa kanzu zao ndi kuzichita zoela kwa mwazi wa mpulumusi.15Kwa ndande ii, ali pachogolo pa mpando wa ufu muwa Mlungu, ndi ampempha uye usiku ndi usana katika nyumba yake ya mapamphelo - iye wapala pamwamba pa mpando ufuma siwatandaze karatasi pamwamba pao. 16Saona njala nchho, kapena lujonchho jwa silalasanchho, wala kutentha kwa kwapyeleze. 17Pakuti mpulumusi wali pakati kati pa mpando wa ufulu wakale owera wao, ndi si wichongoze katika malo yatweka maji, yotamicha, ndi Mlungu wafute kila msozi katika maso yao.''

Chapter 8

1Nthawi mpulumusi wadamasula chidindocha saba, kudali ni kukala chete kumwamba ngati nusu saa. 2Pambuyo midaona angelo saba aima pachogolo pa Mlungu, ni adapachidae mbetete saba.3Angelo mwina wadaje, wagwililila bakuli la dhahabu ili ndi ubani, wanina pamadhabahu. Wadapachidwa ubani wambili dala kuti wauchocho pamoji ni mapempholo okulupalila onchhe katika madhabahu ya dhahabu pachogolo pa mpando wa uyulu. 4Mauchi ya uja ubani, pamoji ni mapemphelo ya okulupalila, yadakwela kumwamba pachogolo pa Mlungu kuchoka mmonja ya Angelo. 5Angelo wadatenga bakuli la ubani ndi wadofalijaze moto kuchoka kuli madhabahu. Pambuyo wadalitaja panchhi, pamwamba pa jiko, ndi kudachokela sauti ya mphambe, mizele ya mphambe ni kutingizika kwa jiko.6Anyiwaja angelo saba anyiayo adali ni mbetete saba adali tayari kupuliza. 7Angelo oyamba wadapuliza mbetete yake, ndi kudachokela vula ya myala ndi moto udasingizikana ndi mwazi. Vidataidwa panchhi katika jiko dala kuli punja yake ipyelele, punje ya mitengo idapyelela ndi mauyu yonchhe ya machomba yadapyelela.8Angelo wa kawili wadapuliza mbetete yake, ndi chinthu ngati pili lalikulu lidali lipyelela ndi moto lidataidwa mbahari. Kumoji kwa bahari kudali mwazi. 9baazi ya viupebe vopuma katika bahali vidofa ndi baazi ya meli zidawanangika.10Angelo wa katatu wadapuliza mbetete yake, ndi nthondwa yaikulu idagwa kuchoka kumwamba, ndii mulika ngati chibatali, pamwamba pa sehemu ya michinje ndi malo yotweka maji. 11Jina la nthondwa ndi pakanga. Upande wa maji udali pakanga, ndi wanthu ambili adaya kuchokana ndi maji yadali yosakome.12Angelowa konai wadapuliza mbetete yake, ndi sehemu ya jua ndabulidwa, pamoji ndi sehemu ya mwezi ndi sehemu ya nthondwa. Kwa icho sehemu ya vonhhe idang'anamuka kukala mdima sehemu ya usana ndi sehemu ya usiku sividali ndi dangalila.13Nidapenya ndi mdavela tai wadali wali kudumisha pakatikati pa jiko, watana kwa sauti yojiwika, Ole, ole, ole, kwa anyiwaja akala katika jiko, kwa ndande yofumuka kupulizidwa kwa mbetete ikali iyo yawandikila kupulizidwa ndi angelo atatu.''

Chapter 9

1Ndipo angelo asano wadamenya mbetete yeke. Ndidaona ndudwa kuchoka kumwamba iyo idangwa pa jiko. Ndondwa idaningi dwa loko paje limapita mjenje lilibe ndimatelo. 2Wadamasula jenje lilibe malile, nimauchi yadakwela kumwamba masafu kuchoka mkati mwa jenje ngati jenje kuchoka pauvuni waukulu. Juwa ndi jiko lidasinda vidi mdima pandande yamauchi yadachova mjenje.3Mukati mwa jenje mzikhe vidachoka kuja kumwamba kwajiko, navojo vidaningichwa mbavu ngati yachipilipi pamwamba pa jiko. 4Widakambidwa osazulu machumba pajika pena mtengo walioje wamachamba penamtengo, pena ikale wandu adalibe chidindo cha Mulungu pamaso pao.5Sadaningidwe mpata yakwapa yao wandu, pena kwatesa pe pamyenzi isano. Utungu wao udali ngati uja olumishwa ndi chipilili yapowaluma mundu. 6Panyengo limenezo wandu safune nyidfa, naimbo sachipata. safune kufa, nambo nyifa siyatawe.7Zige adalingana ndi falasi adaundalidwa kwa ngondo mmutu mwao kudali ndi chindu ngati taji ya zahabu ndi pamaso pao zidali ngati zawandu. 8Adali ndi machichi ngati yaakazi ndi mano yao yadali ngati yamkango. 9Adali ndi mutima ngati mutima yachwua ndi mau vyamapapiko yao idali ngati mau yama khali yambili yaichondo ndi falasi atamanga kupita kungondo.10Adali ndi michila iluma ngati chipilili, pamichila yao adali ndimbavu ya vulu wandu pa myezi isano. 11Adali nayo ngati mfalume pa mwamba pao angelo ajenje uibe matelo, jina lake pa kieblaniya Abadoni, ndi chiyunani wali ndijina a Polioni. 12Ole yo yamba yapita. Penyani kudabwa pa mbuyo paili kuli ngozi ziwili zibwela.13Angelo wa sita wadamenye mbetete yake, ndi nidavela mau ndichoka pa mbepete pa mazabau ya zahabu iyo ili pachongolo pa Mnungu. 14Mau yadakumbila angelo wa sita uyo wadali ndi mbetete asiye angelo anai yao ama ngidwa pamchinje waukulu u Efrata.'' 15Angelo waja anai adali waandaa randawi imene yo furika, siku limene, mwezi umene, ndi chaka chocho, adasidwa afe selusi yawandu.16Unyiji wapolisi yao adali pamwamba pa falasi idali 200, 000, 000. ndidavela idadi yao. 17Chocho ndicho wadaona falasi pa ndoto za nga ndiwaja adakwela mmwamba mwego vifua vao vidali vofuwila ngati moto, buluu yakupwa ndi njano yosopya, mitu ya falasi vidalingwa ndi mitu ya mikango, ndi mkamwa mwao mudachoka moto ndi mauchi ndi salfa.18Ochepa awandu yao adapa ndi yayo mapingo yatatu: moto, mauchi ndi salfa iyo idachoka mkamwa mwao. 19Pakati mbavu ya falasi idali mkamwa mwao pao ndi michila yao -- pakuti michila yao idali ngati njoka, ndavidali ndimitu ili idatumika kwatila vilonda wandu.20Wandu adakala, waja adali sadafe ndivipigo ivi sadatubu vichito vao ivo vidali achita ndipo sadabiye kupembela majini ndi nyundo ya zahabu, ndalama, shaba, myala ndi mitengo - viduivo sivikoza kupenya, kuvela pena kwenda. 21Ndipo sada tubu kupa kwao, ufuti wao, chingololo chao pena njila zao za ungungu.

Chapter 10

1Ndeyapo ni daana angelo mwina wamkulu ndi wachika panchi kuchaka ku mwamba. Wadamangidwa mkati mwa mtamba, ndi kudali ndi mtawalozi wa vula pamwamba pa mutu wako. Pamasa pako padali ngati jua ndi myenda yake idali ngati nguzz za moto. 2Wadegwililila gambo la ling'ona pakati pa janja lake ila lidamasu lidwa, naye wadaika mwendo wako wa kwene pamwamba pa nyanja ni mwendo wake wa humanjele pamwamba pa mtunda.3Ndoyapo wadapaza sauti ya pamwamba ngati simba yapowanguruma, ndi nyenga yapowa dapaza sauti mphambe saba zidanguruma. 4Nyonga mphambo saba yapazidanguruma, ni makaribia kulemba, nompha ni davela sauti kuchaka kumwamba ndii kamba, ''Penyelela ikhale sirichija ambacho mphambo saba zakamba. Usida lemba.''5Ndeyapa angela uyani da mwana waima pamwamba pa nyanja ni pamtunda, wadakwela manja yeke pa mwamba pa kumwamba, 6Ndikulapa kwa yuja waumaya wamuyaya kwa muyaya uya wa malenge dwe kumwamba ndi vanche vilipo, mjika ndi vanche vilipo, ndi mnyanja ndi vonche vilimo: ''Siku kala kuche dwancho. 7Nampha pakati pa siku ija, nyengo wa saba yapasi wa karibia kubula tarumbeta yake, ndeyapo siri ya Mulungu si kale ya yakwanila, ngati umawadafangaza kwa atumiki wake orosa.''8Sauti iyandidavela kuchaka kumwamba idani kambilanchi: ''Pita, tenga gamba lalingana ilo lachakulidwa ambala kika mkati mwa janja la angelo uyowaima pamwamba pa nyanja ndi pamwamba ppamtunda.'' 9Ndeyapo ni dapita kwa angelo ndi kumkambila wani ninkhe gombo lalingana. Wadani kambila, ''Tenga gomba ndi udye. Silichite mimba yaka ikale ndi uchungu, namphala mkati mwa mkamwa mwako silikale lakama ngati asali.''10Nidatenga gombo lalinagana kuchoka kujanja la angelo ni kuliidya. Lidali la koma ngati asali mkati mwa mkamwa mwanga, nampha baada ya kudya, mimba yanga idali ndi uchungu. 11Ndeyapo baadhi ya sauti zidani kambila, ''Ufunika na kurasancha kuhusu wanthu ambili mmaiko, lugha, ndi mafumu.''

Chapter 11

1Nidapachidwa nchungwi ya kuitumikila ngali mpulu wa kupimila nidakambidwa, ''Choka ndi ukapime hekalu la Mulungu ndi madhabahu, ndi anyiwajha alambila mkati mwake. 2Nampao usadapima malola selila kubwalo la hekalu, pakuti apachidwa wanadhu amayiko. Siauponde mujhi oyela kwa nyengo ya myezi arobaini ndi yawili.3Sinikupacheni amboni wanga awili malamulo ya kulosa kwa nyengo ya masiku 1, 260, avala magunia.'' 4Anyiyawa amboni ndi mitengo iwili ya mizeituni ndi mitolonji iwili ivo vaima pachogolo pa ambuye ajhiko. 5Ngati mundhu waliyenche siwalamule kukuwanangani moto kuchoka mkamwa mwao ndi kuwawananga adani wawo. Waliyanche wafuna kunuwanangani nditu wapendwe kwa njila iyi.6Anyiyawa amboni akoza kumanga mitambo kuti mvula isanyencha nyango ndi alosa. Alindi mphavu ya kung'anamwila majhi kukala mwazi ndi kulitimba jhiko kwa lala mtundu wapigo nyengo yaliyonche akafuna. 7Nyengo yaposiakale amaliza dimboni yujha mnyama wachoka mjenje lopande potela siwachite ghondo kupitila iye siwashinde ndi kuwapa.8Matupi yao sigone mta wa mujhi wa ukulu (uwo chifanizi utanidwa Sodoma ndi Misri) uwo ambuye wao adatalamichidwa. 9Kwa masiku yatatu ndi nusu amojhi kuchokela mwa achabale wa wanthu, ntundu, mkambo ndi kila jhiko siapenye matupi yawo ndi siachocha lamulilo kuikidwa mmanda.10Anyiwajhi akola mujhiko siakondwe kwa chifuko chao ndi kukondwa, ingakele kutumilana mphaso kwa ndande anyamcheo olosa awili atapwela anyiyowo amakala mjhiko. 11Nampho pambuyo pa masiku yatatu ndi nusu mphumu ya kupuma kuchoka kwa Mulungu siyalowe nawoncho siaime kwa myendo yao. Kuofyecha kwa kukulu si kwagwele anyiyawo wawona. 12Ndipo siavele mkuwo wa ukulu kuchoke kumwamba ndi yakambila, ''Majhani kuno!'' Nawo siapite kumwamba kwa mitambo, nyongo adani wao ndi apenya.13Mwa saa imeneyo sikalepo ndi chintingiza cha chikulu cha ndhaka ndi imojhi ya kumi ya mujhi siigwe wandhu elfu saba siapedwe mwa chintingiza ndi ya wosia kalile amoyo safyechedwe ndi kumpacha ulemelelo Mlungu wa kumwamba. 14Ole ya kawili yapita. Penyani ole ya katatu ikujha msanga.15Ndipo angelo wa saba wadatimba mbetete yake ndi mkuwo waukulu udakwanicha kumwamba ndi kunena, ''Ufumu wa jhiko watokola ufuma wa ambuye watu ndi wa Kristo wake. Si walamule osata ndi osata.''16Ndipo mikota ishirini ndi anayi yawo adali akala mmipando mwachifumu pa chongolo pa Mulungu adangwa achinawene panchi pa mphumi zao kwatama panchi, nao amamphembhela Mulungu. 17Adanena, ''Tichocha mayamiko yata kwaiwe, ambuye Mlungu mlamutilo pamwamba pa yonche uyo ulipo ndi uyo adalipo, kwa ndande watenga mphavu yako yaikulu ndi kuyamba kulamula.18Mayiko adakwiya nampho, lamulo lako latokujha. Nyengo yafika kwa akufa kulamulidwa ndi iwe kuwapachambhaso otunuka wako olosa, okulupalila ndi anyiwajha adali ndo chipwembwezi cha jhina lako, wonche awili asafanikite chindhu ndi alindimphavu. Ndi nyengo yako yafika ya kuwa wananga anyiwajha yawoo adali nkuwananga njhiko.''19Ndipo hekalu la Mulungu kumwamba lida nukulidwa ndi pokosila chipangano chake tidaonekana mkati kwa hekalu laiye. Kudasi ndi miali ya dangalila, mapokoso, kululuma kwa mphambe, chimtingaza cha ntaka ndi myala ya vula.

Chapter 12

1Ishara yaikulu idaonekana kumwamba: wamkazi uyowadavinikilidwa ndi jhu ndi wadali ndi wadali ndi mwezi phanji pamyendo yake nditaji ya nthondwakumindi ziwili idali pamwamba pa muthu wake. 2Wadali ndi mimba ndi wadali wamalila kwachifuko chamapwetekechue yakubala - katika uchungu wa kubala.3Ndi ishara ina idaonekana kumwamba: Penya kudali ndi njoka yofumila yaikulu ambaye wadili ndi mitu saba ndi nchiwa kumi, ndi wadali ndi taji saba vidali mmuthu mwake. 4Mchila wake udaguguza theluthi inoju ya nthyondwa kumwamba ndi kuzita ya panchi pajhijo, njoka idaima pachogolo pa wamkazi uyo wadali pafuphi kubala ili kuti nyengo wabala, wapate kummeza mwana wake.5Wadambala mwana, mwana wa mmuna, ambayo siwalamule majhiko yanche kwa chiboko cha chichulamwana wake wadanyakulidwa kumwamba kwa Mulungu ndi kumphando wake wa enzi, 6ndi wamkazi wadathamangila kunjikani, pamalo ambapo Mulungu wadali waandaa malo, kwachifuko chake wakoze kuhudumilidwa kwa siku 1, 260.7Chapano kudali ndi nkhando kumwamba. Mikaeli ndiangelo wake ndi adabulana ndi yujha njoka naye njoka wamkulu ndi angelo zake wadabula na nao. 8Nampho njoka wadalibe mphavu za kukwana kushinda. Kwachimwecho siwadalipo ncho nafasi kumwamba kwa chifuko chake angelo wake. 9Njoka yaikulu -- yujha njoka wa kale wamatenidwa ibilisi au satana ambae wadanyenga - jhiko la mphumphu wadataidwa phanchi kupitila jhiko, ndi maangelo wake adatai dwa phanchi pamoji nae.10Potela nidavela sauti ya ikulu kuchoka kumwamba chipano wokovu wajha, mphavu - ndi mfumu wa Mulungu wathu, ndi malamulo ya Kristo wake. Pakuti oshitaki wambele wathu wathaidwa phanchi ambae wadashitaki pa chogolo pa Mulungu wanthu wana ndi usiku.11Adamkosa kwa mwazi ya mwana wambelele ndi kwa mau la ushuhuda wao, kwa mathesiadakonde sana malamidwe yao, kufa. 12Kwa chimwecho, shangiliani, anyaimwe mwamba, ndi onche mkala mkati mwake nampho ole wa jhiko ndi ndihasira yoipha kwa chifuko wajhiwa kuti walindi nthawi ya ufuphi pe.13Nyengo njoka yapowajhiwa kuti wataidwa pamchi kujhiko, wadamchota wamkazi ambae wadali wabala mwana wammuna. 14Nampho wamkazi wadapachidwa mapaphiko yawili ya tai wamkulu, ili kuti wakoze kurumpha mpaka kueneo ilolidalembedwa kwa chifuko chake kujha kuja ngwani, malo ambayo wadakakoza kusungidwa, kwa nyengo nthawi ndi nusu nyengo - pamalo yaposiwakoza kupafika mmeneyo njoka.15Njoka wadamwaza maji kuchoka mkamwa mwake ngati mchinje, ili wachite gharika kumuyanguza. Nampho nthaka idamthamgatila wamkazi. 16Idachakula chikamwa chake ndi kumea mchinje uwo wadalavula njoka kuchokela mkamwa mwake. 17Pothela njoka idamkwiila wamkazi naye wadachoka ndikuchita nkhondo ndi uzao wake - onche anyiwaja atii lamulo la Mulungu ndi kugwililila ushuhuda kuhusu Yesu. 18Pothela njoka idaima pamwamba pa mchenga pamtunda wa nyanja.

Chapter 13

1Ndipo wadachiona chinyama nichichoka mnyanja. Chidali ndi nchiwa kumi ndi mitu saba. Pakati pa nchiwa zake padali ndi kolona kumi, ndi pakati pa mutu wake padali ndi mau yodelela kwa Mulungu. 2Ichi chinyuma nidachiona ngati nyalubwe. Myendo yake idali ngati dubu ndi mlomo wake udali ngati mkango. Ijha njoka idampacha mphavu, ndi pakati pake pa mpando wa enzi, ndi malamulo ene mphavu kupunda ya malamulo.3Mutu wa chinyama chimojhiwapo chidaonekana chili ndi chibampha chachikulu icho chidakachiticha nyifa yake. Nampho chitampha chake chidalama ndi jhiko lonche lidazizwicha ndi lidamchata chinyama. Ndipo adaitamanda njoka, ndande wadachininkha mphavu chijha chinyama. 4Adachitamanda chinyama nacho, ndi adaendekela kukamba, 'Yani ngati chinyama? Ndi ''Yani menyane nae?''5Chinyama chidapachidwa mlomo kuti chikombe mau ya kujhiyelekela ndi matukwano. Wadalamulidwa kukhala ndi malamulo kwa myezi arobaini ndi iwili. 6Chimwecho chinyama chidamasula mlomo wake kukamba matukwano pakati pa Mulungu, wadalitukwana jhina lake, malo yayo wamalama ndi wajhiha alama kumwamba.7Chinyama chidalamulidwa kuchita nkhondo ndi yaoadavomela ndi kwashinda. Tena wadapachidwa malamulo pakati pa kila khamu, wanthu mikambo ndi maiko. 8Onche alama pajhiko samtamande iye, kila mmojhi uyo jhina lake silidalembedwe, kuyambila kuumbidwa kwa jhiko, pakati pa chithabu cha umoyo, icho ni cha mwana wa mbelele, uyo wadachinjidwa.9Ikakhala waliyonche wali ndi sikio ndi wavechele. 10Ikakhala mmoji wa watengedwa mateka ndi kwene mateka siwapite. Ikakha mmojhi wao siwaphe kwa upanga, kwa upanga siwapedwe uku ni kuthela kwa kupola ndi kuembekeza ndi chikhulupi kwa yao alioela.11Tena nidaona chinyama chinjake nichijha kuchokela pakati pa jhiko. Wadali ndi nchiwa ziwili ngati mbelele ndi wadakamba ngati njoka. 12Wadalangiza malamulo yonche pakati pa chinyama chijha choyamba pakati pa kukhala kwake ndi kuchita pakati pa jhiko ndi waja alamamo adachitamanda chinyama chijha choyamba, yujha chibampha chake chalama.13Wadachita vozizwicha va mphavu, ndi wadachita motoo uchike pakati pajhiko kuchokela kumwamba pamaso pawanthu, 14ndi kwachizindikilo wadalamulidwa kuchita, wadanamiza anyiyao akhala pajhiko, wadaakambila kukonja chifani fani, kwa ulemu wa chinyama icho chidapwetekedwa ndi chikwanje, nampho walama.15Adalamulidwa kuchocha mphumu kwa chifani fani cha chinyama kuti chifanifani chikhoze kukamba ndi kuchiticha onche wajha adakana kuchigwandila chinyama apedwe. 16Ndipo wadalamula kila mmojhi, walibe kulemekezeka, ndi wamphavu, olemela ndi mmphawi, fulu ndi kapolo, kulandila chidindo pakati pa jhanjala kwene kapena pamphumi. 17Idali yosakhozekane kwa kila munthu kuugulicha kapena kugula ingakhale wa chizindikilo cha chinyama, ndi ii ni namba iyo iwakilisha jhina lake.18Ii ifuna ulemu. Ikakhala waliyonfhe wali ndi kujhiwa, msiye wakhose kuchita esabu ya namba ya chinyama. Mate yake ni namba ya binadamu. Namba yake ni 666.

Chapter 14

1Nidapenya ndi nidaona mwana wa nkhosa waima pachogolo panga pamwamba pa pili la Ziyoni. Pamoji ndi iye adalipo 144, 000 alindi jina lake ndi jina la atale wake talembedwa pamaso pao. 2Nidavela sauti kuchoka kumwamba imaveka ngati kululuma kwa maji yambili ndi ngati sauti ya mphambe sauti nidaivole ngati atimba vilimbo naimba ndi vilimbo vao.3Ndi aimba nyimbo ya chapano pa chogolo pa mpando waulamundi, pachogolo pa alindi moyo anai ndi okota palije wadakoza kujiyaluza nyimboyo, ingakale 144, 000 adagulidwa pa jiko la panchi. 4Anyiyawa nda anyi, yao saadajideche ndi wachikazi adajisunga asachite chigololo, anyiyawa nde amchata mwana wa nkhosa kila uko wapita, agulidwa mwa wanthu vipacho voyamba va Mlungu ndi mwana wa nkhosa. 5Mkamwa mwao siudaoneka unami, pakuti alibe ukadili.6Nidaona angelo mwina, ndi wanimpha pakati kati pakumwamba, wali ndi utenga wa kumwamba, waalalikile yao akala pajiko la panchi, ndi kila jiko, ndi kila fuko ndi kila mkambo. 7Wadakamba kwa sauti, tokozani Mlungu ndi kumkuzika pakuti nthawi yake yolanga yafika, mlambileni iye wadachita kumwamba ndi jiko lapandu, nyanja yaikulu ndi maji yosachakamila.''8Angelo mwina wadahatila wakawili ndi kukamba wagwa, wagwa Babeli muji uja waukulu, matende uda yamwecha maiko yonche mvinyo ya mphwai ya chiwelewele chake.''9Mwina angelo wakatatu - wadaachata, ndiwakamba kwa sauti munthu walionche, wakalambila chinyamacha ndi chosepa chake ndi kulandila chidindo, pamaso kapona pa janja lake, 10iye naye siwamwe mu mvinyo wa mphwai ya Mlungu, iyo yakonjedwa po sasingizaae ndi maji mu kapu ya mphwai yake, iye siwavutichidwe ndi moto wa chibiliti ndi pamaso pa angelo oyera ndi pamaso pa mwana wa nkhosa.11Ndi uchi wa kupwetoka kwao ukwela kumwamba muyaya ndi muyaya, alije chimwemwe usana ndi usiku amene achilambila chinyama ndi chasepa chake ndi kila uyo walandile udindo wa jina lake. 12Yapande pali udikililo wa oyera, anyiyao agwila malamulo ya Mlungu na chikulupi cha Yesu.''13Nidavela sauti kuchoka kumwamba, ikamba lemba mbasa akua yao akufa mwa ambuye kuyambila chapano wakamba.'' Mzimu, apumulile pa mavuto yao pakuti vichito vao vichatana nao.''14Nidaona mtambo oyera, ndi pamwamba pa mtambo ume ne wakala mmoji chifanizo cha munthu, wali ndi chisoti cha ulemu cha gotide kumutu ndi chisenga chakutwa mazanja mwake. 15Angelo mwina wadaja kuchoka mu hekalu ndi kutana kwa sauti yaikulu kumkambila yuja wakala pamtambo, tenga chisenga chako nyumbe kukolela, pakuti nthawi yo kolola yafika, vokolola va jiko la panchi vapya.'' 16Yuja wadali pa mtambo wadapiticha chisenga chake pamwamba pajikola panchi, jiko la panchi lidakolo ledwa.17Ndi angelo mwina wadaja kuchokela hekalu kumwamba me wadali, ndi chisenga chakutwa. 18Angelo mwina wadaja kuchoka kumadthabao, ndi angelo wadali ndi lamulo la moto. Wadamtana kwa sauti yaikuchi, angelo wadali ndi chisenga chakutwa tenga chisenga chako ukuse nthwi zenche za zabibu pakati zabibu za jiko la panchi zapya.''19Angelo wadapeleka chisenga chake pa jiko la panchi ndi wadakwa zabibu za jiko la panvhi ndi kuponya mpipa lalikulu la mvinyo wa mphwai ya Mlungu. 20Chochezela mvinyo chidadimbidwa dimbidwa kubwalo kwa muji, mwazi udachoka muchochezela. mbaka.

Chapter 15

1Tena ndidaona ishara ina kumwamba, yaikulu ndi iye kudabwicha, kudali ndi angelo saba yao adali ndima pigo vgo saba yayo yadali mapingo yote la (pakati paya asilla ya Mulungu idadi yalolenswa).2Ndidaona chija chida chitika kukala nyanja ya bilauri iyo adasingizana ndi moto, ndi idaima pambepete panyanja yapo waja adali akoza kuposa ya vinyama ndi sanamu yake, ndi pamwamba pa namba iyo iwakilisha jina lake. Adali agwililila vinubi ivo adaningidwa ndi Mulungu.3Adali ndiaimba nyimbo ya Musa, otumidu a ndi Mulungu, ndi nyimbo ya mwana ngosa: ''Njito zako ndi zazikulu ndi zoda bwicha, ambuye Mulungu, nimilila vonje okulupililika ndi njila zako ndi za uzene, mfumu wa jiko. 4Yani siwalepele kukuopajitwe ambuye ndi kulikuta jina lamu? Pakuti imwemweka ndi oyela. Oyela yonje siyanje ndi kupembela pachongolo pako pandande ndi wabwino ndi vichito vako vajiwikana.''5Pambuyo pavindu vo ndidapenya, ndi pamalo poyela, kupunda, yapo padali ndi hema pa uzene, iyo idamasukila kumwamba. 6Kuchoka pamalo poyela kupuma ada bwela angelo saba yao ali nimipigo saba, avala njake zabwino, kitani zilizo wala ndi mshipi wazahabu kuzungulila vifua vaa.7Mmoji wawaja ali ndi umoyo anai adachoka kwa angelo saba mbale saba za dhahabu yayo yadajala pwai ya Mulungu mwene kulama muyaya ndi muyaya. 8Pamdo poyela kupunda kudafala mauchi kuchoka kuli ufulu wa Mulungu ndi kuchoka kulindi mbavu zake pali beata mmoji wadakoza kulowa mbaka mipigo saba ya angelo saba yapoyadata.

Chapter 16

1Ndida vela sauti yaikulu kuchaka kumaloko ela ndi ikamba kwa anyiwaja angelo saba, ''Pita ndi ukamwaze pamwamba pajiko mabakuli saba ya kuipila kwa Mulungu.''2Angelo a yamba wadapita ndi kumwaza bakuli lake pakati pajika; makhavo yaipa ndi yapweteka kupunda ya daja kwa wanthu ali ndi alama ya chinyama, kwa anyiwaja amba adaguwadila chosepa chake.3Angelo wa kawili wadomwaza bakuli lake pakati pa nyanja; idali ngati mwazi wa munthu uyawafa, nde kila chilengedwa cha moyo pakati pa nyanja chidafa.4Angelo wa katatu wada mwaza bakuli lake pakati pa michinje ndi pakati pa chemuchemu za maji; zidakhala mwazi. 5Ndidavela angelo wa mmaji ndiwakamba, ''Iwe ndi okhulupalika - mmaji ulipo ndi uyauliko, oyela kwa chifukwa waja ndi malamula yaya. 6Kwa chifukwa waja ndi malamula yaya. Kwa chifukwa udamwola mwazi wa okhulupalilando oraso, wanikha anyiiwa kumwa divai ndi mwali; ndeicha cha afa.'' 7Ndidavela mazibau ndiijibu, ''Etu! Mbuye Mulungu mwene kulamula pa mwamba pa vonche, lamula zakandi zauzene ndi za malinga.''8Angelo wa kanai wadomwaza kuchaka ku bakuli lake pa mwamba pa jua, lndi lida ninkhidwa ruhusa kupyeleza wanthu kwa moto. 9Adapyeleze dwa kwa kufunda kwa kuofyache, ndi adali pepula mau la Mulungu, mwene mphavu pamwa pa mapigo yanche. Siadalape walakumminkha iye chitu kuko.10Angelo wa kasana wada mwaza kuchaka ku bakuli lake pakati pampanda wa enzi wa chinyama, ndi mdima udauvi ni kila ufumu wake. Adatafuna mana kupitila kupwete kedwa kupunda. 11Adamtukana Mulungu wa kumwamba kwa chifukwa cha kupwetekedwa kwao ndi makavu yao, ndi adakali mkuondekela kusia kalapa kwa chija icho uchita.12Angelo wa sita wadamwaza kuchoka kubakuli lake pakati panmchinje wa ukulu, Frati, ndi maji yake yadauma ili kukaza ku andaa njila kwa mafumu anyi yawasiaje kuchoka kumashariki. 13Ndi daana mizimu itatu ichafu iya idaanekana ngati virwe vichaka kubwala kwa mlama wayuja njoka, chija chinyama, ndi arasa amthila. 14Ndi mizimu ya viuta vichita ishara ndi kudabwicha. Amapita kwa mifumu apajiko loche ili kukaza kwa kusenya pamaji kwa nkhando pakati pa siku ya ikulu ya Mulungu, mwene kulamula pa mwamba pa vanche.15(''Penga! Nitakuja ngati mkhungu! Bala yuja walimba pakati pa kesha, watuza nchalu zake ili siwadakoza kupita kubwala maliseche ndi kuona nchoni yake.'') 16Wadaja nao pamaji kupitila malo ya datanidwa kupitila kiebrania Amagedoni.17Angelo wa saba wadamwaza kuchoka kubakuli lake kupitila mitamba. Nde ya pa sauti yaikulu idavekela kuchoka paela ndi kuchaka kumpanda wa enzi, ndi ikamba, ''Yatha!'' 18Kudali ndi miyale ya dangalila la mphambe, hulindima, vishinda va mphambe, ndi kutinthemela kwa ofye cha - kutenthemela kwa kukula kwa nthaka ambaka si kudawahi kuchokela pajika tangu wadamu alipo pa jiko, mchimwecha ndi kutenthemela kwa kukulu kupunda. 19Muji wa ukulu adangawanika kupitila malo ya tatu, ndi miji ya maika idagwa. Ndeyupo Mulungu wadamkucha babela wamkulu, ndi wadamnikha muji umonea chikambe iche chida jala divai kuchaka kukuipidwa kwake uko kwa punda.20Kila tidwa lidatai kandi mapili siyadaonekane ncha. 21Vula yaikulu ya myala, idali ndi uzito wa talanta, idachika kuchoka humwamba pamwamba pa wanthu, ndi adampepula Mulungu kwa mapigo ya vula ya myala kwa chifukwa lijapiga lidali loipa sana.

Chapter 17

1Mmoji wa angelo asano ndi awili wadali ndi mikate isano ndi iwili wadaja ndi kundi kambila, maja sindi kulangize chilango cha mkazi yuja wa dama wamkulu wakla pa mwamba pa maji ya mbili, 2iye mafumu apa jhiko la panchi achita nae chihololo ndi pa mwamba pa vinyo ndi chigololo chake akala pa jhiko la panchi ajiwichidwa.''3Mngelo wadanitenga chimzimu mbakana kupululu, ndidamwona wa mkazi wakala pa mwamba pa nyama yofuwila uyo wadaja la maina ya wanthu. Nyama yo idali ndi minthu isano ndi iwili ndi nchiwa khumi. 4Wamkazi wadavekedwa mchalu ya mlangali ndi zofuwila ndi kukondwechedwa ndi golide. Miala ya nthungo wa patali, ndi ngale. Mmanja mwake wadagwililila chikho cha golide chajala vinthu voipicha ndi zonyasa ndi chiwelewele chake. 5Pamaso pake padalembedwa jiuma la chisinsi BABELI WA MKULU MAVI WA ACHIWELEWELE WONCHE NDI VINTHU VOIPICHA THIKO LA PANCHI.''6Ndidaona kuti wamkazi yuja wadali walojela mwazi wa a Kristu anyiyao afa ndande ya Yesu, nthawi ndamwona, ndidali munthu wakudabwa kupunda. 7Nampho angelo adandikambila adande chiyani udabwa? Sindikukambila mate ya wamkazi ndi nyama waitenga ( Chinyama chija chili ndi minthu isano ndi iwili ndi zija nchika khumi).8Chinyama udachiona chidalipo, chipano polibepo nampho walipafupi kukwela kutuluka pa jenje lopande potela, ndi siwaendekele kuwananga, anyiwaja akala pa jhoko, anywaja maina yao siyadalembedwe mchikalakala cha umoyo chiyambile mmayamba mwa jhiko sadabwe kuiona nyama iyolipo, kuti palijepo chipano, nampho walipafupi kuja.9Pafunika njelu ndi kwencha. Mitu isano ndi iwili ndi maphili ya sano ndi ya mili yayo wamkazi wamakhala pamwamba pake. 10Nayoncho nde mafumu asano ndi awili, mafumu ya sano yagwa, mmoji walipo ndi mwina wakaliosafike, yapo siwaje, siwakale nyengo yochepa.11Chinyama icho chilipo, nampho chipano palibepo iye naye naye ndi mfumu wakanai nampho ndi mmoji wawaja mafumu asano ndi amili, ndiwapita kuwananga.12Zija nchiwa khumi udaziona ndi mafumu khumi yao sadaulandile ufumu, nampho salandele udindo ngati mafumu pa nyengo imoji pamoji ndi chinyama. 13Anyuiyawa ganizo lao ndi limoji, ndisamphache mphamvu zao ndi lamulo chija chinyama. 14Sauyambane ndi mwana wa mbelele, nampha mwana wa mbelele siwapambane ndande ndi mbuye wa mambuye ndi fumu wa mafumu, ndi ndande ya uje tidatanidwa, tidasakhidwa achikulupi.''15Mngelo wadandi kambila, ''Majhi udayaona, paja wadakala yuja wachigalolo ndi wanthu, makamu, mitundu ndi mikambo.16Zija nchiwa khumi udaniona zimenezo ndija nyama samwipile yuja wachigololo, naoncho samchite kukhala opande changalalo ndi maliseche, samudye thupi lake ndi salibuche moto. 17Pakuti Mlungu waika mmitima yao kutunga dala lake pakuwana kuti nyama ya ipachidwe mphamru zolamula mbakana mau la Mlungu yapo silikwanile.18Yuja wa mkazi udamwona ndi mujhi okulu ulamulila mafumu ajhiko.''

Chapter 18

1Paubeyo pa vinthu ivi nidanuvona angelo mwena ndiwachika panjhi kuchoka la kumwamba. Iye wadali ndi malamulo ya kulu, ndi jhiko lidayelechedwa kwa ulewelelo wake. 2Wadalila kwa mukuwo wa ukulu, kunena, ''Wagwa, wagwa ujha mujhi waukulu Babeli! Wala malo yakala viwanda, ndi malo ikhapo mizimu yoyipa, ndi malo akalapo kila kadri ndi mbalame yokwiicha. 3Pakuti mayiko yonche yamwa mvinyo okumbila chiwelewele chake uwo umpelekela kulamulidwa. Mafumu wa jhiko achitanchigololo ndiiye. Ogwile malonda ajhiko alianchuma kwa phavu ya ukolo wake wa kukumbila.''4Ndipo nidavela mkuwo wena kuchokela kumwamba ndi venena, ''Chokani kwaiye wandhu wanga, kuti msadajha kugwilizena mwa machimo yake, ndi msadajha kulandila mapigo yaiye yonche. 5Machimo yake yajhala pamwemba ngati kumwamba, ndi Mulungu wayakumbukila yocheta yake yoyipa. 6Mlipeni ngati umowadakupila wena, ndi mkamlipe mara kawili kwa umo wadichitila; mwa chikombe ichowadachisingizana, msingizilanena mara kawili kwa chifuno cha iye.7Ngati uino wadajikweza iye mwene, ndi wakukala, kwa kukumbila, mpachene mavuto yambili ndi chidandaulo. Pakuti wanena mtima mwake, 'Nakala ngati wamkozi wa mfumu; wala osati oslidwanwali wa muna; ndi wala sindiona chililizi.' 8Kwa icho mkati kwa siku limojhi mapigo yake siyamlemeche. Ntifa, chililizi ndi njala. Siwapelezidwe kwa moto, pakuti ambaye Mulungu ndi wamphavu, ndi mlamulilo wake.''9Mafumu ajhiko adachita chigololo ndi kuwanangidwanjelu pamojhi ndiiye sialile ndi kumchila chililizi yaposia uone unchi wa kupya kwaiye. 10Siaime papatali ndiiye, kwa kuopa mapwete kechedwe yaiye ndianena, ''Ole, ole kwa mujhi wa ukulu, Babeli, mujhi uli ndi mphavu! Kwa ntawi imojhi lamulo lako lajha.''11Ogwila malonda ajhiko lilani ndi chililizi kwa chikuko chake, pakati palijhe ata mmoji wagula malonda yake ncho - 12malonda ya dhahabu, ndalama, myala ya mtengo, lulu, kitani cha bwino, zambarau, hariri, yofiwila, ntundu wonche wa mitengo ya mtengo ya kunungila bwino, chombo cha njhiwa ya ndovu, kila chombo cha konjedwa kwa mitengo ya mtengo, shawo, chichulo, mwala, 13Mdalasini, viungo, uvumba, manemane, ubani, mvinyo, mafuta, ufa, wabwino, ngano, ng'ombe ndi mbelele, farasi ndi magari ndi otumikwa ndi mizimu ya wandhu.14Vipacho ivowavikumbila kwa mphavu za imwene yachoka kuchoka kwalwe. Kukumbila kwako konche ndi mapambo yachoka, siyapezekanancho.15Amalonda avindhu ivi yawo adapeza ulemelelo kwa chikondi chekeswaime papatali kuchoka kwa iye kwa ndande ya mandha ya mapwete kedwa ya iye, ndialila ndi mkuwo wa chililizi. 16Ndikunena, ''Ole, ole mujhi ujha waukulu wavekedwa kitani chabwino, zambarau ndi kufuwila, ndi kupambidwa kwa othahabu, ndi vito vya ntengo ndi lulu!'' 17Mkati mwa ntawi omojhi ulemelelo wenche umeneo udachoka. Kila oyendecha wa meli kila baharia ndi wonche wanamajhi ajhiko ya kubandarini, adaima papatali.18Adalila yapoadauwona wuchi wa kupyelela kwa iye. Adanena, ''Nimujhi uti ulingana ndi mujhi uwa waukulu?'' 19Adataya malifumbi mmwamba mwa mitu yawo, ndi kulila, ''Ole, ole mujhi waukulu pamolo ponche. Yawo adali ndi meli zawo mnyanja ya ikulu adali olemelele kuchokana ndi vyuma vawo. Mkati mwa ntawi imojhi wawanangidwa.'' 20''KOndwani pamwamba pake, kumwamba, anyiimwa okulupalila, atumei ndi olosa, kwa mate Mulungu wapeleke langidwe lanu panewamba panu!''21Angelo mwene mphavu akaimiwa mwala ngati mwala okulu wa kupepelela ndi wadalitaya mnyanja, yaikulu wadenene, ''Kwanjila iyi, Babeli, ujha mujhi waukulu, siutai dwe panchi kwa kunyinyinala ndi sidonekana ncho. 22Sauti ya vinanda, wanamuziki ocheza filimbi ndi mbetete siavekancho kwaanyiimve. Ingakale fundi wa ntundu waliwonche siwawone kana kwa anyiimwe. Ingakale sauti ya ntondo sivekelancho kwanyiimwe.23Dangalila la nyali siuchochadangalila mkau mwaiwe. Sauti ya okwata ndi kukwatiwa sivwkwlancho mkati mwako, pakuti amalonda ayiwe adali wakulu akulu ajhiko, ndi amayiko, anyengedwa kwa ufiti waiwe. 24Mkati mwake mwasi wa olosa ndi waokulupalila udaonekana ndi mwazi wa wonche adapedwa pamwamba pajhiko.''

Chapter 19

1Pambuyo pake vinthu ivi nidavela sauti ngati yamlio waukulu wakundi lalikulu la wanthu kumwamba idakamba, ''Italeluya, wokovu, chitukuko, ndi mphavu ni va Mulungu wanthu. 2Hukumu zake ni za zene ndi lakweli, pakuti wamlamulo kahama wamkulu uyo waiwananga jhiko kwachiwewele chake.''3Kwa mara yakawili adakamba, ''Haleluya mauchi yachoka kwake miuyaya.'' 4Anyiwaja midala ishirini ndi anai ndi viumbe amoyo anai adagwada ndi kumwabudu Mulungu wakala pamphando wa enzi. Adali amakamba, ''Amina. Haleluya!''5Ndiyapo sauti idachoka kumpando wa enzi, idakamba, ''Muyamileni Mulungu watu, anyaimwe atumiki wake onche, anyaimwe mumjiwa iye, onche alibe umuhimu ndi ali ndi mphavu.''6Ndiyapo nidavela sauti ngati sauti ya kundi la likulu la wanthu, ngati sauti ya ngurumo la maji ya mbili, ndi ngati ngurumo la mphambe, imakamba, ''Haleluya! Ambuyeni Mulungu wanthu, mtawala pamwamba pa onche, kwatawala.7Ndi tishangilie ndi kusangalala ndi kumpacha chitu kuko kwa chifuko ukwati ndi sherehe yamwana wambelele wajha, ndi bibi aukwati wali tayali.'' 8Wadaluhusidwa kuvekedwa kitani chabwino ndi iye chophulikila (kitani chabwino ni vinthu va uzene kwa waumini).9Angelo wadakamba nane, ''Yalembe yaya atukuke anyi yao alalikidwa kusherehe ya ukwati ya mwana wambelele, 'Chimchijha wadanikambila, ''Yaya ni mau yauzene ya Mulungu.'' 10Nidagwada pachogolo pa myendo yake nidamwabudu, na mpho wadanikambila, ''Usidachitha chimwechiline ni mtumiki mnjako ndi wabale wako anyiao agwila uzene wa Yesu. Mgwadile Mulungu, pakuti uzene wa Yesu ni mzimu.''11Potela nidaona kumwamba kwa achakuka, ndi penya kudai ndi falasi oyela! Ndi yujha wadali wamkwela watanidwa oaminika ndi wauzene. Lamulo kwa uzene ndi kuchita ukhondo. 12Maso yake ni ngati mwali wa mwana, ndi pamwamba pa munthu wake wali ni taji ya mbili wali ndi jina ilolalembedwa pamwamba pake ilosiwajiwa munthu waliyonche ingakale iye mwene wake. 13Wavala chivalo ichochabizidwa katika mwazi, ndi jina lake wadatanidwa mau la Mulungu.14Majeshi ya kumwamba yadali yamamchata pamwamba pa farasi oyela, adavekedwa kitani chabwino, choela ndi chokadwa. 15Kukamwa kwake udachoka upanga otema ambao ku yaangamiza mataifa, nae siwatale kwa chiboko cha chichulo, nae kuponda vyombo za divai kwa hasira kali ya Mulungu, kutawala pamwamba pa onche. 16Nae walembedwa mwamba pa chivalo chake ndi katika faja lake jina, MFALUME WA WAFALUME NDI AMBUYE WA AMBUYE.17Nidamuona angelo waima jua. Wadatana kwa sauti yaikulu mbalame zonche arumpha kumwamba, ''Majani sonkhani pamoji kuchakudya chachikulu cha Mulungu. 18Majani mdye nyama ya wafumu, nyama ya majemedali, nyama ya wanthu ya wanthu onche, alihuru ndi akapolo, alibe mate ndi ali ni mphavu.''19Nidamuona mnyama ndi mfumu wa jhiko pamoji ndi majeshi yao. Adali ajipanga kwa chifuko chakuchita nkhondo ndi mmoji uyo wadakwela phunda ndijeshi lao. 20Mnyama wadagwilidwa ndi nabii wake wamthila uyowadazichita alama katika kukalapho kwake. Kwa alama izi wadanyenga anyiwajha adalandila chapa yamnya ndi anyi yao adagwada chosepha chake. Onche awili adataidwa akali amoyo katika ziwa la moto liwako kwa chiberiti.21Anyiwajha adakhala adaphedwa kwa upanga uwou dachoka mkamwa mwa mmoji uyo wadakwela phunda, mbalame zo nche zidadya mizoga ya mathuphi yo.

Chapter 20

1Pambuyo pake ndi deona ongelo ni wachika kuchokela kumwamba wali ndi kii la jenje lilije patelani chingwe cha chichulo cha chikulu mmkoja mwake. 2Wadachogwira chija chwajoka njoka ya kaleka mme onyenga kapena shetani ndi kumanya vyaka elufu. 3Wada afaya nyenje lilije potela wada limanga ndi kuwilale chichundo pamwamba pake. Ichi idali chimwecho dalakutifi wadanyenga waduapajiko chapamondo mpaka vyaka maelfu yapofivitele pambuso pako siwa fichilidwe kwa ntawi yochepa.4Pambuyo pako ndido penya mipando inene ido kalidilwa ndianyiwaja adopa chidwa ufumu alamulilo mmemoncho ndi daona malo ya anyiwaje adodulidwa mito kwa chifuko cha linizo la Yesu ndi kwa mau lamuhungu anjio si ado mkulupalile chintu kapena nkope yake nchiade kna kulandila chisongezo pamwamba pa nkope zo pakena mmanja mwao ado mwamte ndele ndi apaufulu olamolila ndi kristo kwa vyaka elfu.5Chamene adamwalita adakalila siada je kumtendele mpaka ntawi uyako elfu yapo vidata kuneneko kuzuko kuyamba. 6Wamwawi ndi walije machimo nde muntu waliyenche mwene watenga malo pakati pa kuzuka kuyambila nyifa yoyamba ilije mpano pamwamba pa wadu ngati chuyiyawa sipakale ndi ope mbeleche ndi opempelo ndi sialamwihile ndi iye pakati pa vyala elfu.7Nfawi vyako elfu yupo sifikile potela safana gwamasulidwe kuchokela mundende mwake. 8Siwapite kubwalo kwanyenga wantu ajiko malo yanai yajiko gogu na magogu kwa bweza pamoji chifuko cha nkondo - siakale ambili ngati mchenga wa nyanja ya mchole.9Adepida pamwamba pa kwawa la jiko naoncho azonguwila gunule wanthu amulungu, muji ukondedwa na nipo mot udabwela kuchokela kumwamba ndi kwawawanga woncho usana ndi usiku siku sonche. 10Setana mmene wada anyenga wada taidwa mkati mwanyanja limene liwala chibiriti, mmene mnyama ndi olota wamnami adakala atotaidwa, sia vutichidwe usana ndi usiku siku zonche.11Pambuyo ndido umwe mpando usungidwa wankaro woyela ndiyuja wadakala pamwamba pake jiko ndimifambo ida fawa kuchoka yapo wadalipo nampo sipada kalepo malo ya anyirwo kupita. 12Ndida wamu owalila onche odashiapavu ndi awene siamafumidwe china pakati pampando wasofa ndi vikola kalanchi vida maswali dwa pambuyo chikala kala chena chida masulisha chikalekale cha umoyo wasata, wautu akufa ade lamolidwe kwa chija chido lembedwa mkati mwachikalakala, kulangiza vija amavichita akali amoyo.13Nyanja idaachocha wando adafa adali mkati mwake. 14Nyifa ndiminda yada achocha wantu ada mwalila mkati mwake ndi wafu ada mwalili ata laawidwa kuchatana ndicho ama chochota. 15Ngati jiko la waliyenche filida pezeke lalembedwa mkati mwachikolakola cha mtendele wasota adetadwa mkati mwa nyanja yamoto.*

Chapter 21

1Pambuyo pake ndidaone mitambo ya chapano pakati mitambo yoyamba ndijiko loyamba zidato kuta ndi nyanja siido koleponcho. 2Ndida ona muju oyela Yerusalemu ya chapano, umeneo udaja panchi kuchokela kumwamba kwa Mulungu, uda kinyedwa ngati wa mkazi wakwati wakonjendwa chifuko cha mamuna wake.3Ndedavela mau ya akuru kuchokela pampando wachiyambilepo ndiukamba, ''Penya! Malo ya Muungu ylipamoji ndi wantu, nayenche siwalame pamojinao. Siakale wanto wake ndi Mulungu mwene siwa kale nao nditiwakale Mulungu wao. 4Siafute msozi wolionche kuchokela pakati pamaso yao, ndi sipakale ndi nyifancho, kapena kupemene sela kopena kulila kapena kupwetekechedwa, nkani ngaizi kale zidato kuyenda.5Iye mmeneyo wadali wakala pamwamba pampando wakalekale wa dakamba, ''Kapenya! Ndi chita nkanizonche kukale za mpoya'' wadakamba liumba ili chifuko nau yaja ndi yazene ndi zeaedi.'' 6Wadandikmbila, ''Nkakwiza yudato kuyenda! Ine ndioyamba ndiotela, kwa wayenche usona, lujo siundi mpache chakumwa popanda malipilo yaliyonche kwalokale pakati mawilidwe yi maji ya mtendele wosata.7Iye siwapambane ndiye siwapeze ulisi wa nkani izi ndisinchi kale Mulungu wake, niyenche sina kale mwamwanga. 8Nampo ngati umo ili kwa wantu amauta, sakwapolila, aipicha, akupa, achigololo afiti abali ndi vinywaji ndi aunami wonche ndi malo yao siyakale myanja ya moto wa chiseriti upyeleza ufi nde nyifa yakawili.''9Mmoji wa angelo saba wadeja kwaine, mmoji mwene wadali ndi mbale saba ya chala vibulilo saba potela ndidakamba, ''Maja pano sindikulangiza wamkazi waukwati wamkazi wa mwanawambelele.'' 10Pambuyo wadanditenga patali pakati pa umoyo kupili lalikunu ndi lalitali ndi wada ndilangiza muji wa vichifo vabwino Yerusalemu, ndi uchika panchi kuchokela kuwamba, ''Kwa Mulungu.11Yerusalemu udalindi venelali wa Mulungu, ndi kukadwa kwake udali ngati alintu chamate ngati mwala waglazi labwilo la yaspi. 12Udali ndi papa lahi kuru lalitali lizi ndi vicheko kumi ndi viwili, pamoji ndi angelo kumi ndi awili mwicheko pamwamba pa vicheko padeli palembedwa majina ya makamu kumi ndi yawili ya wana wa izulael. 13Mbaliya kuzambwe padali ndivicheko vitato mbali ya kumwela vicheko vitato mbali ya kumpopo vicheko vitatu ndi mbali ya pakati vicheko vitatu.14Mapopa ya muji idali ndi msingi kumi ndi lwili ndi pamwimbapake padali ndi majine kumi ndi yomwili ya otuwiki amana wambelele. 15Mmoji wadakamba ndiine wadali ndi chipimo cha chiboko chida konjwedwa kwa dhahabu chifuko cha kuyezela mojo vicheko vake ndi mapupa yake.16Muji udaikwidwa mkati mwa mwiba utaliwake udali ngati upana wake wada upima muji kwa chipimo cha chiboko stadia 12, 000 kwa machilali (utali wake, upana indi kimo vidali ngana). 17Mmwemoncho wada yeza pupa lake kujimbala kwake kudali chila 144 kwa maezedwe ya chimuntu (ndivimanencho vipimo va angelo).18papalida mangidwa kwa yaspi ndi muji uli ndi mpwahi ya bwino, ngati grasi lambwino. 19Msingi na pupa udali wa ikidwa kila mtundu wamwela wachuma cha thamani. Oyamba udali yaspi wakawili kidali yakuti samawi ndi ya katatu lidali kakedon ndilakanai zumaridi, 20loka sana sardoniki la sita akiki la saba krisolitho, ndilanane zabarajadi la tisa ya kuti ya manijano ndila kumi krisopraso la kumi namoja hiakintho lakumi nambili amethi stoi.21Vicheko kumi nchiviwili idali golodi kumi na mbili chicheko chilichonche chida konjedwa kuchokala golodi imoji nopita mwamuji mudali golodi ya bwino ndii ionekana ngati grasi labwino. 22Sindidaone mmalo mopempelela mkati mwamuji pakuti Mulungu mme wa imilila pamwamba pavonche ndi mwana wa mbelele nde mope mpelela mwake.23Muji si ufuna jua kapena mwezi dala kuwalicha pamwamba pake chifuko ufuru wa Mulungu uda wala pamwamba pake, ndi nyari yake nde mwana wa mbelele. 24Maiko siyaende kwa kuwala kwa muji umeneo mafumu wajiko siapeleke kujichita kwao mkati mwake. 25Vicheko vake sivimangidwa ntawi ya usana ndi sipakala ndi usiku paja.26Siapeleke kujifufumula ndi ndemu wa maiko mkati mwake. 27ndipolibe chinyalala sichilowe mkati mwake kapena wali yonche mwene siwachite chintu chilichonche cha manyasi kupena kunyenga siwalo ikapanda mujiwaja achamene ma mejinayao lalembedwa mkati mwa chikabhole cha umoyo cha mwana na mbelele.

Chapter 22

1Mara angelo wadamilangiza mchinje wa maji ya umoyo, maji yadali yomelemeta ngati bilauli. Yadali ya moto tililika kuchoka katika mpando wa chifumu cha Mlungu ni cha mpulumusi. 2Kupitila pakatikati pa mtaa wa muji. Katika kila kona ya mchinje padali ni mtengo wa umoyo, ubala mitundu kumi na mbili za matunda, ni mubala matunda kila mwezi. Machamba ya mtengo ni kwa chifuko cha ufulumusi wa maiko.3Wala sipakala ni laana yaliyo nchenche. Mpando wa chifumu wa Mulungu ni akumtumikila wake amutumikile. 4Amwone nthope jakew, ni jina likala pamwamba pa vipaji va sura zao. 5Sipanata ni usinkuncho; wala sipakale ni kufuna dangalila la yaa au juu kwa ndande ambuye Mulungu amulike kwa anyiio. Nao atawala muya yani muyaya.6Angelo wadanuikambila, ''Mau ya yani yokulupalilo ni zene. Ambuye Mulungu amitima ya mlose ada mtuma angelo wake kwalangize otumina wake chichokele pafupi yapa.'' 7''Penya! Mkuja chisanga! Wadalisifwa iye walemeleza mau ya ulose wa chikala kala ichi.''8Ine, Yohana, niuje nidaveta mkupenya mambo yaya. Yapo mdavela ni kupenya midagwa panchi namwene pachogolo pa myendo ya angelo ni kulambila, angelo wadamilangiza mambo yaya. 9Wadani kambila, ''Usaita chimwecho! Ine ni oyumina njako, pamoji ni abale wakoaolosa, pamoji ni anyiwaja alemokeza mau ya chikala ichi. Mlambila Mulungu!''10Wadanikambila, ''Wayaika alama mau ya ulose wa chikala kala ichi, chifuko nthawi yasendelela. 11Uyo walije haki, naendekele kutokala wala ni haki. Wali oyela, ni waendekele kukala oyela.''13''Penya! Nikuja chisanga. Kulifidwa kwanga kulipamoji ni ine, kumilipa kila mmoji kulingana ni icho wachita. 12Ine ni Alfa ni Omega, oyamba ni Otela kuyambo ni kutela.14Adalisidwa anyiyao achapa mchalu zao dala kuti apate haki ya kuja kuchoka katika mtengo wa umoyo ni kuulowa muji kupitila mmakomo. 15Kubwalo kuli galu, afiti, achigololo, ukupa, olambila vasepa, ni kila wakonda ni kutangatila kukamba va unami.16Ine, Mpulumusi, namtume angelo wanga kupanya ni kuhusu mambo yaya kwa nyumba za pamphelo. Ine ni wachigololo mbadwa wa Daudi, nyota ya umawa iwalaja.''17Mzimu ni okwatiafwa akamba, ''Maja!'' Ni uje wavela wakambe, ''Maja.'' Waliyonche walini lujo, ni wajo, ni waliyoncha wakumbila, ni pate maji ya umoyo chabe.18Nimukambilila munthu navela mau ya ulose wa chikala kala ichi: Ngati waliyondke waongezela katika yameneyo Mulungu wamwengezela kubulidwa yalembedwa katika chikale kala ichi. 19Ngati munthu walujoneke akuyachoche mau ya chichala kala ichi ulose, Mlungu wachoche malo yake katika mtengo wa umoyo ni katika mji oyela ambayo nkani zake zalembedwa mkali mwa chikalakala ichi.20Iye wayapanya mambo yaya wakamba, ''Efu! Nikuja chisanga.'' Amina! Maja mpulumusi. 21Mwawi wa Ambuye mpulumusi mkale ni kila munthu. Amina.